A Chilima amema a Malawi kupita ku zionetselo

Advertisement
Saulos Chilima

…chipani cha DPP chikhumudwa nawo

Wachiwili kwa Mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima anauza a Malawi kuti apite ku zionetselo pa 13 December chaka chino.

A Chilima ananena izi mu mpingo wa katolika ku Lilongwe. A mpingo wa katolika anayika pa zolengeza zawo nkhani yopempha ma membala a mpingo wawo kupita ku mseu kukaonetsa mkwiyo wawo ati poti a boma akuchedwa kukamba nkhani ya malamulo a kavotedwe.

Saulos Chilima
Chilima: Pa 13 December, tiyeni mukamatche.

Pa mpingo wa St Patricks umene a Chilima ndi membala, iwo ndiwo anapatsidwa zolengeza kuti anene.

Atafika pamene mpingowo umadziwitsa ma membala awo zopita kumseu, iwo analengeza.

“Pa 13 December, tiyeni mukamatche. Muzavale yunifolomu ya Tchalitchi,” iwo anatelo.

Anthu ena otsatila chipani cholamula cha DPP ati akhumudwa ndi khalidwe la a Chilima amene amamema anthu kugalukila boma lawo lomwe.

“Izi si zoona anachita a Chilima, mesa iwo ndi gawo limodzi la boma? Tsopano iwo sakanatha kupempha kuti asanene zolengeza? Apa sanaganize bwino,” anatelo wina otsatila DPP.

Advertisement

154 Comments

  1. That’s True ngat chilima samamema anthu kut apite kuziwotselo why being on that position of announcing? Kunalibeko ena akanalengeza? Chilima is people you may know in Dpp

  2. ka tsamba aka ndi ka anthu amisala, iwe walembawe uzivere mtolo muziyamba mwafufuza nkhani musadatumize ngati ndi ndale zakukanikani

  3. chilima sanalakwitse,nanga ukanakhala uthenga woipitsa chipani cha MCP mukanati alakwitsaso kupanga zolengeza??? mmmmmmmmmmmmm asiyeni achilima

  4. Present your story in the right order please. He was just presenting the letter by the PAC which he was asked to read in church.

  5. Chilima was at church as a catholic member and not a government delegate, He had two things to choose, God or DPP. If you were in that situation what could you have done? Leaving God to serve a political party?

  6. Malipota apa Malawi,why do want to comfuse the nation chilima anawerenga kalata ya ma bishop. Or iweso ukanatha ukanatha kuwerenga ukanapatsidwa mwayiwo….kupusa

  7. Chilima akuziwa kuti Ku dpp kulibe Chaka chifukwa cha Bushiri atenga zithu zake ndiye alindimaganinzo opita chipani chosusa mcp ,Moto wambiri chilima

  8. Mmmmhh! Ntchito Zolembana Pachibale Ndichomcho Olo Ulibe Zozienereza, Chilima Anangopasidwa Zot Alengeze Ndipo Amaenera Kutero Bac Nde Inu Nkhaniyi Simukuidziwa Mukuthamanga Kuzaisia Apa Mmmm! Simukutha Ntchito

  9. ACHILIMA ANAITHA ….SIKULAKWA KUWAUZA ZA MADEMO IWOSO NDIZIKA ALINDIUDINDO MBALI YAO POFUNA KUTETEZA UFULU WAMALAWI NT ZOFUNA ZAmuNTHU MODZI OR 100 kusiyana ndi 17mn plus …….

  10. a DPP ali busy kuyankhula chingelezi, akuti “This is unprofessional!” eeeh this is Bullshit”! eeh mwakuti mwakuti….. kkkkkk Muona kuti mupanga bwanji, mbwenu musovenge

  11. This is poor & unproffessional reporting at its highest level.Again,this is uncalled for media reporting! Mind u,was Chilima authored the epistle?He jst pronounced what the letter contained.What if it was another person without a name like Chilima perhaps who read out the letter,wud t hav gone up to this far?I beg to differ plz.Do the investigative journalism.Otherwise,Malawi won’t progress wth this nosensical reporting!!

  12. Koma Vuto Ndi Chani Apa, Chilima Amapemphera Akudzi Chomwe Akuchita, Ena Amapembedza Ndale Chifukwa Azikhumudwa Nazo, Koma A Dpp Akuopa Chani Kt Bill Ya Zisankho Akambilane, Ngakubadi Anthu Eti,

  13. Amadziwa zolengeza munthu umawerenga kaye sikuti iyeyo Uliya muhiti ongonyamula kalata osawerenga podziwa kuti izi mwina ndambali yanga siziyenda adakakana,koma iye anapitiliza kulengezabe,ndimwana oukira mbuyache full stop

  14. Anthu timathamangila kuyankhula molakwika mofulumila mwina, posowa kupanga chiganizo poti kuganiza kusiyana, nkhaniyi achilima sanamemeze amalawi kuti azapange zioneselo pa 13 ai, Iwo amawelenga zomwe zinalembedwa ndi adindo ena komanso msikulo olengeza za mumpingo anali Iwo, osati zimachoka mmutu mwao ai Iwo anali ngati mdindo oziwisa anthu za nkhani tisamasemphanise zinthu kuti tiziika ena mmau osiyanasiyana mwina izi zinachitika mwadala kuti chikalatacho chinalipo koma China go sung idea mcholinga choti tsiku la achilima lolengeza azalengeze Iwo mcholinga chofuna kuona kuti kodi angalengeze? koma simaganizo ao ai tiyeni zonse tiisiile mulungu tisaweluze potinso tonse tikudikila kuweluzidwa.

  15. Iyeyo sanawameme anthu kukupanga ziwonetsero ayi koma amawerenga zolengeza koma ngati mumadana nawo kambani nkhani ina,kumbukirani komwe mwachoka,musamale pofuna kutumiza mauthenga anu,a malawi tikuona

  16. Achilima ndimuthu odziwa ndale apa aziwa kale kuti iye Ku DPP kulibe chake mdipo mtsogoleri wathu ndibola panyani mbuzi yachabechabe

  17. Chilima sanameme anthu inu pilizi. Chilima awelenga kalata yolembedwa ndi ma Bishop…awelenga OSATI amema. This is vague, silly and stupid reporting. Kufuna kuti anthu adane basi. Wakhuta mbewa

  18. Please anyone making comment should make it short, so we professional comment readers (PCR) will be able to Read all comments. Thanks for making our work easier!!

  19. It wasn’t wrong hence he was told to give the church announcement as a church member also one of the Gods servant. Let’s put aside political affiliations. In church we don’t do politics but to do what is the best fr the pple. If anyone feel digress on his speech m its we running away fr the track . Theirs a place where we can do politics, even in parliament, pple can fight but when they are out, they meet at a common goes , leave him alone .

  20. Actually he was just reading a statement that was addressed to general public,he said not in his own words but according to the letter he was reading.are you dumb???

  21. Atolankhani a chimalawi amalemba zamutu mwawo ,pompa mudalemba zoti MCP imaba madzi zochitsiru basi tamalembani zomwe zachitika bwanji musaiwale kuti ena amakhala kumudzi amafuna azidziwa nkhani zomwe zikuchitika osati zamabodzazi

    1. Kodi a 24 simachite manyazidi muja mnkati MCP illegal water scandal? Illegal connection amayika poyera yera anthu akuona ndi maso? MCP imakutsegulani mmimba? Simunati kkkkkkk maboza basi! Manyazi bwa?????

  22. If people were not consulted on this bill which people? If Chiefs has come out with this issue it means people were consulted. The best way just call for a referendum so that everyone has a chance of expressing their opinions.

  23. Kumva ndi kumvesesa ndiziwiri zosiyana,wapanda za mademo ndi Chilima?,iye anapezeka kuchurch ngati opemphera pachurch po,osati ndiyemwe akuza anthu zademo.Muzapusa nazo zinthu zokumva mmalo momvesesa.

  24. Koma anthu ena chilungamo chimawasowa munthu amuwerengesa za mu mpingo nde mumvekere amakopa anthu ha ha ha uyu nde azamva kuwawa 2019 azanenanso kuti amubera backward never forward ever

  25. Chilima sanameme anthu,wangowerenga uthenga, even abusa ngakhale atakhala achigololo ayenela kuwelenga ma chapter oletsa kuchita chigololo.

  26. kd munthu umakawelenga pagulu usanapange kaye tchek uyu akunama watenga ndale zake wakalowesa mumpingo bwana pita mthamangiseni uyu ndikapilikon akanakhala kt nd wa dpp sakanawelenga uthengau monga munthu wamkulu akanadziwa kt kungowelenga kokhako ndichisokonezo mdziko chonde amalaw pewan zionetsero zolimbana nd boma kumafa anthu osalakwa pt boma siligonjela munthu apolice mufufuzen chilimayu akufuna kuyambisa chisokonez mkwizingen asaphese ana anuwake fotsek

  27. No that’s bull sheet! Zabodza izi. Musamuyike mau nkamwa Chilima kodi inu Malawi 24 munakhala bwanji? You are too much gossiping kodi mwasowa cholemba?

  28. more fire Chilima and this is a move he knows what is he doing sikuti samadziwa nanga every Sunday amawerenga Ndi Chilima? if the answer is no and why only this Sunday?

    1. Gama Phiri you are right,,they are playing a mind game,,,they knew kuti muzolengeza muli nkhani yamademo,that’s why anampatsa kuti awerenge,,Chilima is a leader,and leaders ali ndi influence,hence anamuuza kuti akhristu akamva akhale ndi chikoka choti akapite kumademo wo,,,,bravo Chilima.

    2. Pembe point of correction chakwera is man of God kungoti vuto la Malawi ndilakuti amaona ngati pastor sangakhale pastor koma mbava, a satanic, achifwamba, oledzera ndiwo adzilamulira dziko

    3. Dziko lili pamoto why pple tiyen tizikangana za nzeru cause these cant help sitingapange zoti tikayende kuonesa kukwiya magesi akuzimiramu pple tiyen tidzuke timamenyera nkhondo ena tikuvutika

    4. Dziko lili pamoto why pple tiyen tizikangana za nzeru cause these cant help sitingapange zoti tikayende kuonesa kukwiya magesi akuzimiramu pple tiyen tidzuke timamenyera nkhondo ena tikuvutika

  29. Sindikuona cholakwa chilichose powelenga ndiye kuti or kuwelenga buku loyela ndikulakwa?chalembedwa chimawelengedwa bola ngati umatha kuwelenga ukakhala wa DPP usamapephele?

  30. kodi zimene mukulemba izi Malawi apita patsogolo??Chjlima amawelenga zolengeza mutchalitchi koma pazolengezapo panali zomema anthu kupita kuxiwonetselo Eeeish atolankhani athu muli kutali kwambili zamanyaz heavy

  31. Malawi 24 bodza chilima sanameme a Malawi kupita ku zionetsero ,komakuti anapatsidwa kalata yo khudza zionetsero kuti awerenge ndipo ananena mwini wakeyo .

    1. amene amawerenga tsiku limenelo anali iyeyu ndiye atambwaliwa anapezerapo mwayi pofuna ku kwaniritsa zokhumba zawo ,pogwiritsa ntchito munthu amene kwa iwo amamuona ngati crowd puller komanso kufuna kubweretsa udani pakati pa sau ndi peter m’malo mobweretsa mtendere.

  32. Poor reporting just to bring Comfusion among pipo,its Catholic Church not Chilima,Chilima was just making Church Anouncements for that Sunday Service

    1. Masamba ,wekhatu ukut radio osati Mpingo kapena Munthu wazorengeza mumpingo.pitan ku khoti mukasumire Catholic & mipingo inayo pomema anthu kukatenga gao pazionesero zapa 13/12/17

  33. thats political spirit we always desire osamangoti yes bwana mzopusa zomwe ng Chilima olo atakuchosa mu corruption family yawoyo uzakhala ndi mbiri ya boh

    1. Iiii….bro u r commenting right things on a wrong report…he just had to read the bishops letter…..not his actual words….mwina akanalankhula on his own on aradio o tv osat kuwerenga kalata mu church…. Thats ur view….

  34. Mbuzi za dpp zingomusiya salalakwitse chilima. this is not the 1st kuti alengeze mu church bwanji simunamuike mu news nthawi imeneyo.

Comments are closed.