Police seek help finding child’s relations

Advertisement

Police in Mzuzu have asked for help in finding parents or relations of a four-year-old child who was involved in an accident in the city.

The child told police that his name is Jomo Chirwa and he stays in Katoto location within Mzuzu City.

Jomo was one of the injured people in the Zolozolo accident which occurred on Tuesday in Mzuzu.

The accident involved OP Bus Services which was on its way from Mzuzu enroute to Mpherembe.

During the accident which left five people dead, Jomo sustained a fracture on his right arm and was rushed to St John’s Hospital by a well-wisher.

Police have since asked anyone with information about the boy or his relations to visit St John’s Hospital or call on 0999436677.

 

Advertisement

34 Comments

  1. Mwana uja abale ake anapezeka thursday 6pm atamva kuti basi yachita ngozi ndipo ena amwalira anapita kuchipatala kukawonako mwatsoka anapeza kuti omwe anali ndi mwana uyu auntie ake amwalira,anamutenga kuti akakhale naye kumudzi mwatsoka nkuchita ngozi

    1. No, here is the full information I got on a Whatsapp News Forum. Copied as it is.

      UPDATE ON JOMO CHIRWA, THE LOST CHILD
      Good morning, am pleased to inform u ladies that amayi ake apezeka. Ndinalawilirako ku St John’s hospital, only to find that his mom has been found. Akuti mwanayu anali ndi aunt ake amapita naye kumudzi. Anachita kuwalilira aunt akewo kuti akufuna akaone agogo ake. Nde mayi ake anamupakilira zovala then ulendo anayamba aunt ndi mwana uja. Ngozi itachitika, mayi ake anayimva dzana koma never thought it could be the bus yomwe anakwera mwana wawo, coz komwe kunachitikila ngozi was totally a different direction to where Jomo was going. Dzulo ati iwo anali kwawo pheeeee, olo kuganizilako zoti angakhale mwana wawo. Nde madzulo akuti mpomwe anamvetsetsa kuti bus imapita towards direction ya kwawo only that inakapezeka uko coz driver amathawa a traffic. Akuti munthu amawauzayo continued to say that koma kuli mwana akusowa makolo, azimayi ati mayi nzathuyu collapsed.. I feel china chake chinawauza kuti ndi mwana wawo. Then they started following up with the father ndi anthu ena, only to discover that it was really him. Afika ku chipatala ko dzulo usiku. But the sad part is that the aunt Jomo was travelling with sakuoneka mpaka pano mtsikana wa Maka 18 imagine. They checked with Mzuzu Central hospital nakonso kulibe. Nde poti nthawi inali itatha, anakapeza kuti ku mortuary atseka, nde akapangako check lero…. Very sad.
      In short, Jomo is safely in the hands of his mother now, the boy is only 2years 9months.

Comments are closed.