Blackouts killing Malawians – MHEN

Advertisement

Malawi Health Equity Network (MHEN) has said that prolonged blackouts are killing Malawians in hospitals.

MHEN says in a statement that ESCOM and Malawi government authorities must know that persistent blackouts that have rocked the country have huge negative impacts on the health sector .

MHEN: Blackouts are killing Malawians in hospitals.

According to MHEN, some patients who were on oxygen died during the time it took to switch on a generator after a blackout.

MHEN has since demanded ESCOM and Malawi government to make sure that health facilities must have electricity for 24 hours.

“We, therefore demand electricity in all health facilities 24 hours a day. No load shedding in lines that connect health facilities,” reads the statement.

Recently, ESCOM said that Malawians will be having electricity for a period of 8 hours per day.

Advertisement

117 Comments

  1. Zatikwana odwala kuchoka chipatala cha Ku dz kumatumizidwa Ku ntcheu chifukwa magetsi azima komaso akukanika kukoza genset ndekulibwino muzagoitenga tisamayione eeeeiiiish

  2. Bombs likuyenera kuyankha mlandu wakupha anthu chifuwa cha magetsi. Mu ulamuliro wa Bingu adasowa ndi Mafuta, lero lino magetsi. Mudatembereredwa?

  3. Amalawi ndi anthu omvetsa chisoni reasoning imativuta,guys chiwelengero cha anthu chikuchuluka omanga nyumba zamagetsi akuchuluka and we are talking about the same generation of electricity since 1993 magetsi asavute?

  4. Thts tru,iwowa mabwana mmakwao magetsi saazima,akadwala amapita kuzipatala zakunja kapena zodula zolipila,even most pple dies 4m curable diseases due 2no drugs/matupi opelewela zakudya zamagulu,matenda amagomaliza basi gwelo la umphawi.

  5. [ WE CALL IT LOVE and YOU CALL IT HATE] what kind of people are you? you do’nt even take to what people are telling you of thelr complents. what ynu should know is that time is fritting little by little you wo’nt be there for good take care. care

  6. If you can ask Dausi that there are blackouts in Malawi . His answer will be:” No. There are no blackouts but there is just a problem of electricity which is cause by past regimes. So we are working on it ….” Minister of Denials

  7. These bamboocraat politicians of Dausi, Goodall, Peter let alone Atupele were born in mud round grass thatched kitchen without electricity and in them don’t care about electricity.. No wonder..

    1. U must fear God and thanks Him, that non of ur family members has meet this problem as of now. oxygen in hospitals can not work without electricity

    2. How many have been killed by electricity? Black out killing people and even also on the other hand electricity are killing innocent people.

  8. Malawi fool heart of africa. Munakana thandizo la bushiri kuti magetsi asamazime mukuti ndi false prophet inu chikukukhuzani ndichani pa u false prophet wake? Osangolandila ndalamazo bwanji ndikuthesa vuto tili nalori.check zambia, south africa,botswana,south sudan analandila thandizo la bushiri pano magetsi sakuthima maiko awo. Koma malawi ndye tikhala chonchi. Pano mukupanga k5000 yogwilana kodi mukuti change tizichitenga kuti. Apa ndye tikamapita ku jon mukutumiza mafumu pa boarder kuti azatibwenza, mugwilizane wina avulala. At the end peter achoke president opanda tsogolo ophesa anthu……

    Kodi zopopa magazi zili pati

    1. How u knw kuti ndizakumidima.inu ndiboma lanu ndye osapita kukatenga zanu kumidimako bwanji. Ife zoti ndizakumidima we dont knw wht we need is electricity not zakumidima zakozo. If u tok abt government 4get boy.anthu angati akuba ndalama zaboma shld we say u dont see that. Ndye boma ndalama itenga kuti yopangila magetsi. Even yesu ali pansi pano amkati simwana wamulungu anthu amenewo ali akuchiza anthu muziwanda koma anazakhulupilira atafa ndi kuuka kupita kumwamba mpamene anthu anazindikila.ndye mukamangosazila kuti anthu akt bushiri ndiwa satanic izo muzasala nokha azanu akuchita bwino.kuweluza ndikwakwe kwa mulungu musileni

    1. nkhani si ya dpp koma ngakhale nthawi ya mcp udf,blackout idzakhalako ndipo inakhalako, onsewa analephela musazitenge ngati enawa ndi angelo,

    2. Inu zot mages anu mumadalila madzi simukudziwa? mudikile mvula iyambe vuto lichepa,kutukwana munthu mupindula chan?

    3. @wathe thats what am saying as a country we are headed for the worst scenario as possible. We should have seen this coming moti muona ngati zinthu zizikonzeka? Escom has never grown as a company koma ma customers. Compare ma consumers a electricity in 2000 and 2017 with a constant supply base and imagine the scenario

  9. Politicians are the main attribute to this Saga,(Escom unnecessary blackouts ) when there is a clear short fall they divert the truth , they blind fold mutharika that things are well under control while there is a stinking cat under the table , we r fed up with this , pathological liars , politicians

    1. Too many procedures involved to purchase things in govt n that’s not even a simple way – ESCOM should step up in their loadsheldings n prevent some importantly places like these

    2. lol whats simple between purchasing a back up power supply and ESCOM preventing loadshelding? load sheldings have been there for years and it seems like ESCOM is nowhere near finding a solution.its just getting worse n worse..soon even ku state house magetsi azayamba kuzima.

    3. Chifundo…i hop u are missing the point here…government is to take the blame…hospitals opperate using government funding called ORT…now what can hospitals do if they are being underfunded by the ruling thieves….where will they get money to buy gensets if they are failing to buy boom for washing beddings for patients???

  10. Malawi wafikapo, no longer a warm heart of Africa, nkhondo kunalibe ija imeneyi, ngozi ziphe anthu, anamapopa aphe anthu, apolisi aombere anthu, matenda , njala umphawi uphe anthu, Mlengi wakwiya , we need intervention

  11. Imagine 24hours no electricity. And someone is busy saying Peter is boma 2019.mxim we will remain like that forever. Its like tonse a Malawi mayi athu ndamodzi

    1. ngakhale kutabwela chakwela mavutowa sangathe.pokhapokha titasintha mindset athu,dzikoli lingofunika munthu ngakhale atakhala osaphunzila koma akhale ndi maganizo aumunthu oziwa chimene akupanga

  12. blackout can’t kill patients in hospitals… kapena pa death certificate akumalemba kut wafa coz of blackouts? am not medical doctor anyway

    1. who is to blame if patients are dying coz of blackouts?? can hospital operate without backup?? tell them to buy genset

    2. Osatukwana pa media. Fid you go to school. Don’t have literal meaning. Read between the line. Don’t use shallow thinking

Comments are closed.