MCP are vampires – Nkasa

Advertisement
Joseph Nkasa

The ruling party wind has once again swayed Joseph Nkasa to employ panegyric tactics, in favour of the governing political body.

The veteran musician who is popular for political songs, speaks highly of the ruling Democratic Progressive Party (DPP) while dressing down Malawi Congress Party (MCP) in his latest song.

Joseph Nkasa
Nkasa: Exposes the dark history attached to MCP.

The song which has gone viral on social media, portrays DPP as a peaceful party which makes it more deserving to be ruling Malawi.

Nkasa strengthens his position through exposing the dark history attached to MCP.

The opening verse begins with a Biblical allusion; he narrates people’s choice of Barnabas over Jesus when they were asked as to who should be granted freedom.

“Lero kunabwera DPP chipani cha mtendere, la chitukuko boma ndi Arthur Peter Mutharika, Anthu ali pa ufulu DPP chipani cha mtendere, misewu ya phula ndi Arthur Peter Mutharika, Chimanga kutapa kutaya DPP chipani cha mtendere, sukulu za luso ndi Arthur Peter Mutharika, olemba nkhani akulemba DPP chipani chamtendere, opanda omangidwa ndi Arthur Peter Mutharika pazifukwa za ndale, DPP chipani cha mtendere,” he sings on chorus.

The song gets ugly for the main opposition party when Nkasa mentions the atrocities that were committed during its rule.

“Pomwe panadulidwa mitengo yaminga, pozaphuka sipazaphuka wa papaya, minga yomweyo ndiyo izaphuke, Fisi akasamuka kupita Phiri lina sikuti kumeneko akasanduka nkhosa, mtima waupandu amayenda nawo, kumbukani chifundo cha nsema mitondo, chinadyesa matumbo ake onse mmimba, Malawi Congress Party ndi ma vampire.

“Zikanatheka kuifusa mizimu, kuti tambala wakuda abwereso, inakakanisisa kwa mtuwagalu.”

This is the third song Nkasa has done in the political realm this year. He started with a public relations song for former Minister of Agriculture Dr George Chaponda in the wake of maizegate, then he produced Yoswa for President Peter Mutharika.

He got into the limelight with political songs during the late Bingu Wa Mutharika’s rule in 2007 with Mose Walero. In 2014 he engineered another political propaganda tune for Joyce Banda.

 

Advertisement

369 Comments

  1. Against all my belief and convictions;

    I think Nkasa have just proved me wrong, … This is one great Malawian artists!

    Just one single product has attracted all these comments, proves that he is a great artist whose products really go to the core of his audience.

    Love him ore hate him his song tickles almost all of his audience.

  2. Kutetedzana? Kkkk anayimba za wakuba mmela uja pano total trash muziona Malawi wake si wadzana uja tikuona zomwe mu kuchita afisi

  3. Tikufuna mechanic odziwa ntchito abwele adzatikonzeleko mutu wa mkasa wafoila (mental mechanic Mm) call me soon after

  4. Nkasa Amapembedza Mafano Musiyeni Akaziona.Nkasa Ndi Munthu wadyera. Nyimbo Zake Sindingagule Bola Ndidzimvera Sir Paul Banda”dzatamanda Ambuye Ondipatsa Moyo”

  5. peter munthalika he is like joe gwaladi or josephy nkasa .musicias who sing song without knowing what they are singing .no wonder gwaladi calls himself a proffesor and mind you muntharika is also a proffesor

  6. What the problem here coz ndiufulu wake mkasa kukamba zomwe akuona kuti ndizabwino kwaiye inuso ingoimbani ngati mukuona kuti paliwina akuchita mofanana ndi momwe mumalingalira

  7. Nkasa kuimba nde waimba ,amene zamunyasa awona kuti apanga bwanji,makutu ndianu

  8. mkasa komwe uliliko undimvere ukumaimba nyimbo kumanyoza anthu mudzina la ndale ukulakwitsa,udzayenda mmanja mwa anthu.anthu omwe ukuwanenewo zimawapweteka akadzakwiya sudzawafuna.

  9. When those vampires come into power you will praise them in your songs just to gain favours because that is what you do with every government, what sort of person are you without direction?

  10. Nkasa galu wamunthu umphawi wamuvuta wangofuna ndalama alibe kalikose pano ndicifukwa adakungenda kunambuma iwe nthwi ya amai

  11. awa anayamba ndi Bakili kenako Bingu lero ndi izi follo 4 leader chifukwa chake anthuwa samasiya zatumbwazi chifukwa cha anthu ngati okomedwa osayankhura zolakwika za munthu kumangokhalira

  12. Nyirenda, Nkasa is talking the truth, Mcp started long time under Kamuzu to be Vampires in Malawi ( Blood Suckers).

  13. Dzulo anali kwa mai lero akut wabweranso ku DPP peter anali poison l as nw ndimunthu waphindu hahaha mkasa xool ndi yabwino koma poti umadziwa kut zabwino kudyera akapusa ndie adyereni

  14. Imwe mwanyithu Mukususka MCP kumbukirani vinthu vyose vikawa mitengo yiwemi nyengo ya MCP muboma mulikunjira vakuba vekha tawina malawi tikusuzgika ivo vikwenda mumiti yawo nkhuba. MCP niboma lakuvwira tawina malawi 2019 MCP

  15. Inu uyu kapena osapota mbava Ndani angasangalale munthu waba chimanga cha amphawi akumudzi kenako mkumayimba Zomuchemelera that’s very stupid

  16. Vuto laumphawi umangochitapo ndizosayenera zomwe… Sorry Mr. Mkasa… Madyera too much. Mumudziwe Yesu ndiakuphunzira ake..

  17. Zoti Nkasa mutu wake sugwira sadziwa ndi ndani kodi nanu,kazingomuonani uyu mwezi uli ku mdima ukatuluka akhala bohbo josey

  18. Nkasa ndi more, osamumvetsetsa onse ndiye ma fools amenewo, anati iye ndi woimba si wandale ndipo amamvera boma lolamura. Kaya atatenge a Mcp azamvera iwo muzingomuyangana basi ndi woimba, mumafuna oimba otukwana boma mpaka boma liziganiza zowapha chonchija eti?

    1. Ndiye nkasa ameneyo, likazagwa azaliimba za mwanonso likumva. Palibe boma lingaganize zokupha oimba ngati nkasa amene amanyadira boma lolamula. Tiyeni timvere boma chisankho chikazafika tizasankhe amene tizawafune.

  19. Nkasa supports government of the day,so do i.bravo Nkasa!

  20. Nkasa oro ineyo sindifuna kuveraso Nyimbo zake adandinyasa adakakhara wina sadakayimba Nyimbo ya mose warero ayiiii Nyimbo yabwino ngati imeneyija koma zose ndi 2019 muva kuti nkasa mwakataya atamugenda zenizeni osati mujamu adamuyerekeza muja ayiiiii komatu sakuremeraso ayi zaziiiiii

  21. Kkkkkk galimoto kagwire ntchito komaso iwe tiyeko mkasa tivote panopa uwerenge makomets ngati pali a darkness Democratic paty

  22. Don’t waste time discussing about useless musician he was there with Muluzi, JB, Bingu and now Peter let’s assume leadership is changing tomorrow he may change as well

  23. Nkasa is just a stupid musician, put your whatsapp numbers ndikutumizileni nyimbo imene inamunena pitala, not ija ya Analila ija

  24. Inu ankasa nde simuzasiya kulila anthu akumenyani mpaka kutope kma mungopemphela kt azingokumenyan asaganize zokubayani ma jekeseni mwamva ankasa? mbuz ya oimba

  25. Mcp ndi Anthu oipa kwambiri akupha asazaloweso boma amenewo tizakhala pamamvuto owospa kwambiri akulu akulu tiganize mofatsa chonde chonde ndagwila mwendo wanu Anthu akhaza awa alibe achisoni azingokhala osusa boma paka paka koma simuzawinaso ndikulumbila mulungu modzi yekha

  26. Xhilungamo akuchiziwa iwe ngati ufuna kutengapo gawo tenga sizo tukwana munthuzo vuto la pampanje ndilimenero uyu akhale Ndani ndichifukwa ndina thawako akuziwana awa (kunxqono kuthula)

  27. mwachidule tingoti mkasa ndi hule chifukwa amakwela imene ikulamula pamenepo even MCP ikaxawina muxamuona mkasa akuimba zochomelela mcp yot anainyoxa .koma opanda mxeru ndi andalewa chifukwa ndikakumbukila mene adainyoxela DPP sibwex ali nayexo

  28. DPP killed Chasowa,Njaunju, and 20 others on July 20,if these are not vampires what are they ? Mind you Nkasa is not a musician, he is a story teller.He started with Bingu kanenere a Police,then a mayi ,Zonse NDA mayi JB,it was all praises with a Mayi,now with President Peter as Joshua,4m contract with Katsonga went sour,Does he know what he is doing ? His stories are for money,that’s all. With MCP 2019_he ll change tune. This is the man we need not to waste energy with,it’s a matter of time.

  29. wokuswa myala lero watola chikwama mmati anganeneso chani abale . Konseko kuopa kubwelera kokaswa myala kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk nde akufuna chintuwisa

  30. Phungu is one of the nonsense people ever… Even chipereni wind has direction but him no where to go. What he wants is to milk funds of poor malawians

  31. Thanks to Dr.momoh who saved and cured me from hepatitis B.. virus. with his herb medicine you can also reached him for similar
    *Or any other….virus…like.. Hepatitis…..C… Virus….
    You can reach him through this number…you can add him on WhatsApp believe me you will never regret it
    +2349068579672
    ​Your cure is here for you​ !!!

  32. komatu munthuyu akunena zoona guy’s, mcp ndi chipani chankhaza chimadyetsa anthu ku ng’ona kugwilila azimayi ndikuba ziweto zamphawi komanso idapha achina gadama mwankhaza powakhoma ndi misomali m’mumu

    1. Mukakhala ndi mtima umenewo sitingapite patsogolo MCP yakale idathera ku chipani cha DPP chifukwa mambala akuphawo anathawira kumeneko. Pano chipani cha MCP chilindi anthu owopa mulungu

    2. Kuopa Mulungu kwake kwa pakamwatu osati mumtima….mudzawona ndiomwewa omwe adzatitafune akadzawina….abible says: no man can please another man except God himself..

  33. sadziwa nkuwerenga awa ndipo wamuuzira mau oti vampire Ndani? Umphawi wamukantha pompano timva ayimba nyimbo praising Bushiri kuti apeze kanganyase kkkkk

  34. Are they? can you prove, I never vote for them and I will never vote for them in the future but I can not call them vampires but rather good friends and my bosses.

  35. Kudana ndichilungamo mukufuna achite zomwe mukufuna inu mwagwa nayo tiye M
    Nkasa DPP ikufuna anthu ngati iwe MCP yaboowoka yaphofomokanso DPP more fireeee

  36. MCP should sue Nkasa for deformation Coz boma linati opopa magazi kulibe so why Nkasa is coming up with these claims ….let him alongosore bwino

  37. chitsiru ichi changotopa ndi maluzi,chamisala osachitengela zake DPP Ikutuluka m’boma 2019 akazabela tizapanga ma demo opanda malire mpaka tizavotaxo anyapapi inu tatopa nanu MCP boma tione zina

  38. guys , possibly admin wa news page iyi akunama.we can just expose our stupidity pomamunyonza munthu yemwe.sanalakwe. ndiyankhabe ndikaimvera nyimbo yo my self. i have smelt a rat in this issue

  39. Koditu Nkasa si munthu oti ndi ali ndi nzeru. Adati si wandale, then ati Mose wa Lero, then adanyoza DPP saying amene akulamulira ndi amayi, then adanyoza boma lilipoli saying a police malipiro sakukondwa nawo, then akuti Joshua wa Lero. Itati ilowe MCP muzamumva akujama ya MCP. Uyu amangofuna ndalama ndi chitsiru munthuyu amasowa zochita. Ine sindikuona chodabwitsa. MCP 2019 boma koma Nkasa ukagwere oyimba athu tili nawo kale.

  40. People are cowards busy accusing Nkasa opusa mbuli inu ainkinu osayimba yanu yasukulu bwanji. We’re commenting coz tamva. Kaduka pa Malawi

  41. eeee……..eeeeeee……eeeeee……eeeeee kma mphuno yake inakalota anakakamba zamzeru bt he need 2 irumminate hs idear,,

  42. Mkasa u r useless clueless and just a wasted talent… You are a shame in the music industry and Malawi at large… You just a boot licker youre greed for money will kill you… You are calling MCP vampires yes they suck ignorance poverty and corruption your thinking has drained like you are a 2015 baby….

  43. We are not kids axe, that time is long gone and we all know it. That’s why you were beaten 5-1 by the so called vampires. You see vampires but we see redemption, meanwhile the clock it ticking.

  44. A nkasa ndichisiru ndipo akuganiza kut a2 angawcthe maganiz ndi dyera lakero? amalawi pan anachangamuka uchisir wakew asapak naw a2 ena

  45. Ankasa ndaninso,garu wa chabechabe. President aliyense amuyimbire nyimbo ndicholinga chopempha ndalama. Bulshit, kang’wing’wi iwe.

  46. Awa school idawadutsa kumanzere ndachitsiru amangipita kulikose komwe akuona ngati kuti akhoza kupezako kanthu mboli yankhuku iyaaaaa

  47. Mcp has to sue him as of now a certain senior chief in the south did say him knows who are begind it and that he can deal with them! So for Nkasa to claim otherwise then he has to prove in the court of law I suppose!

  48. I don’t see the reason of betraying one another while truth is uncovered. Stop to dig over our ear drums with your speechless accusations

  49. It doesnt matter spellings capture his content of words. Amalawi tidatani kodi? aati ifeyo ndiye odziziwisitsa vizungu, bwanji ngati tafikapo why

  50. unaimba kale mkasa nyimbo ina yake yoti wanunkha malawi tilowera kt under the same leadership of peter ukumukwezay ndie tidakadikirab kt mutiuze kumene tilowele

  51. wsh nditayandikana nawe wa masaya akuluwe, tisazakuone uli khwekhwerekhwekhwere ndi ma vampire ukutinenafe titatenga boma 2019 with clean sheet, kaya akutuma, akupweteketsa ameneyo, n dziwa kut zopepera zakozo zikungoonjezera molalo ku MCP, koma a DPP ngat iri pressure ndiye muzakomokatu 2019, tambala wakuda more fire

  52. Nkasa is one of the visionless musicians who do not have actual direction. And I believe he even do not know what he does.

    1. Opanda vusion ndiiweyo,aliyense amayang’ana chakudya chapakhomo lake ndiye mkasayo ngati podyera pake mpamenepo musiyeni mkomwemkomwe a mcp mukuilimbikirayo anthu sanaiwale mwina ma born 4 nu ndiamene mungamaombe mmanja poti mumangova kma kadxina kameneka koti m……c…….p kanationetsa zoipa kuposanso mautsogoleri mukunenawa,mwina chakwera adakasintha dxina lachipani koma ichi cha 31years anthu tikumangidwa nyakula fukwa ulibe ndalama yamsonkho kapena card lau membership very sad

  53. Kodi nkasayu waiwala zomwe tinamupanga ku Dowa? Pa nsomkhano wa Amai Funso langa kwa nkasa ukufuna kuphwanyidwanso MUTU

  54. Kkkkk characters of pple in dpp and its acosiates : KULI ANTHU OPHUNZIRA KWAMBIRI,KOMA NDI OPEPELA OKHA OKHA…chisanzo aliyense akuchidziwa KULINSO MBURI ZAMBIRI ZOMWE SIDZIZIWA CHOMWE ZIKUPANGA…the likes of nkasa ndi chisanzo…

  55. UMPHAWI NDI UCHIMO LERO NDAMVOMELEZA NDITHU Kodi mkasa osamutengela ku mental hospital ngati muja mukumuchitira wandale Vincent uja bwanji???? Uyuso ndi openga kaya ngati simukudziwa mumutengele pa chiyambi myimbo zake zinali ndi matanthawuzo omveka bwino koma chama 2010 myimbo zake mukabvera bwino bwino mundibvomeleza kuti mkasa akudwala misala ndi openga akufunika thandizo la chipatala mwansanga asayambe kugenda anthu ndithu

  56. DPP ndiye ya ma vimpire.kupopa magaz.kupha achi albino.kuvulaza otsutsa boma.then ma vampire mndan.umbuli ankasa unakuphan.ku mcp suzalandilidwa ase ngat umakwera boma ku mcp malo suzapeza

  57. Munthuyo adzafela zaeni ake pajatu adayimba nyimbo yonyoza Peter Mutharika pamene amakodzekera iye za kapeni m’chaka cha 2014.

  58. Opempha can do anything to please the giver……….. pitilizani kulidyera boma. Otherwise the truth mukuchidziwa

  59. If you ate tired if singing Nkasa just go kwanu ku Machinga ukapumule. What you are singing is tosh and absurd, what you are praising in your song was done by a line of presidents from Kamuzu, Muluzi, Bingu and partly Joice, what have Peter done so far to be recognised as a good leader rather than shielding corrupt government officials? Stupid Nkasa.

  60. munatha inu ankasa munali kale simuthaso kuimba nyimbo zanu ine ndikuntha zaka pafupifupi 10 osavela amene umawatamandawo sakutenga mkomwe kukankhala zochitika kusonyeza kuti ulibe luso lamaimbidwe uziona 2019 inu ma vampireyo akulowa m’boma

  61. kodi iyeyo tanthauzo la vampire amalidziwa kapena wangoneneramo??,,,,anamapopa dpp,,kupha ma alubino dpp so who are the vampires here??,,,,the opposite is really true

    1. Eeeeh boss kuchipha chizungu cha Queen Elizabeth kkkkkkkk mpaka raw model kkkkkkk koma sukulu za naiti eeish sizinthu. Tabagulisami ma memory card anyimbo kale za malume bokosizo mwakacheremu kkkk

  62. I used to respect Nkasa but he has turned out to be a stupid political musician. As Malawians, we should learn to give creidit where it’s due; those who tarnished the image of MCP are in DPP now. Who killed Njauju, is it MCP? How about Chasowa, Mbendera and the 20 striking civilians in Mzu and this is happening during multiparty time. KUBA in all ministries, the blackouts, drug shortages, water scarcity and Nkasa wants Malawians to keep on clapping hands for DPP no!!! that’s madness…………….

Comments are closed.