We were lucky to lose by-elections – DPP

Advertisement
Francis kasaila

The ruling Democratic Progressive Party (DPP) has described its loss in the October 2017 by-elections as a blessing.

The party has said the loss was an opportunity to clear the mess within the party before 2019 polls.

Francis kasaila
Kasaila the loss is a blessing.

The sentiments come at a time when critics have warned the party that a defeat in the by elections is a sign of what will happen in the 2019 elections.

But DPP spokesperson Francis Kasaila said the loss is a blessing in disguise as it will help the party to clear its image to the public.

“Ndimwayi ndithu chifukwa chatipasa mpata kuunika kuona kuti ndipati pamalakwika (It is luck because we now have a chance to know where we made mistakes).

“Mulungu watikondera kuti tiluze by-elections kusiyana ndi general elections (God has favoured to lose the by-elections rather than general elections) said Kasaila.

Kasaila further challenged opposition Malawi Congress Party (MCP) that the DPP will win the general elections in 2019.

“Iyi inali friendly match, ife yathu ndi league yomwe titenge (This was just a friendly match, we will win the league,” he said.

The 17 October by-elections were held in three wards and three constituencies and the DPP emerged victorious in only one ward.

Advertisement

162 Comments

  1. Thanks to Dr.momoh who saved and cured me from hepatitis B.. virus. with his herb medicine you can also reached him for similar
    *Or any other….virus…like.. Hepatitis…..C… Virus….
    You can reach him through this number…believe me you will never regret it
    +2349068579672
    ​Your cure is here for you​ !!!

  2. A DPP amisala awa… aziluza kumene… iya aluzanso 2019 atikwana azipita… boma lautsiru ngati ili sitinalione… chinzibambo chiachukuluchi nde chili pheeeee…. za ziii

  3. The only solution that APM can do for nation it’s to fire all cabinet members and Put up the new team that can deliver.He shud start with you the rotten Kasaila.DPP has failed in areas especially in Public service delivery and good governance. If you think dat dat I’m joking just check their campaign manifesto.

  4. These guys are great losers , we all know that the defeat is a clear sign that DDP is gradually going home , u r not telling the truth to u sleeping master , pple are simply done with DDP , i can smell a mass DDP exodus to MCP and UDF very soon , there is nothing gud left for you corrupt niggars , #Nankhumwa is one of such an exodusee , he has lost his case to #JB , gold diggers

  5. hohohohoooooo.uko kunali kulira kwa anamfedwa a DPP.tsopano tiitana amfumu achakwera atiyankhule kenako tinyamule malilowa.mwambo ndiomwe uja kkkkkkkkk

  6. Guys, stop insulting the leaders in DPPor MCP.We need constructive comments and criticisms. Our politicians are fathers and mothers at home.please learn to respect them.

  7. munthuyu kasayilayu ngwa mwano kwambiri. Uwuso ndi mwano kuti kuluzaku ndi bwino. Mukuwona bwa? uyu akamayankhula ndi mwano wokhaokha munthuyu. Amalawi atopa nanu basi ,chifukwa olo mukhoze zinthu pano zizangokhala za kanthawi kochepa ,nthawi ya kampeniyi basi kwinaku tizayamba kulilaso ndi musatitole mwanvaaaaaaaaaaaaaaaa?

  8. It is absolutely the meaning of checks and balances in multiparty system. Citizens have opportunity to express opinion and views through the ballot. The most important is vote for candidates who are honest, responsive and hardworkers for their communities. Once mistakes are done, wrong choice will cost the general population. This is why people must scrutinize candidates before giving them a vote. Know your candidates by checking background, employment histrory and their achievements. This will lead to general community develpment.

  9. dpp is a strong party and will win in 2019.koma zoti aliyense kulamura ndi mbuzi zomwe nde ndi zachamba.we want leaders to rule.osati anthu ambuu avala blue azitilamura zopusa kumachita mwano.adalamura ndani kuti filling station amange pankhomo la bwaira hospital. izi zinakwiyitsa anthu ku chilinde and area 23.mapeto ake kuluza chisankho.kuyankhula zopsetsa mitima anthu.chose the best to speak on behalf of the party like malemu kudotoni (mhsrip) and zina ndi zina but mcp cant outsmart the mighty dpp which will win with 69 % in 2019 bbecause of the sound and sweet leadership of apm.inflation down to 8%.roads and infrastructure development. bwana osanyoza munthu.chipani chokhala ndi kulemekeza azimayi.other parties dont have women in its high polibro.shame.go go dpp to 2019 victory

  10. The funny thing about our cabinet is that, it has been put on a microscope. It’s too small to read the minds of all who are involved. And it’s surpring to hear such statements from one spokesperson him or Dausi. Where do they get the energy for doing that?? Dpp this time is too disgraceful out of rotten membership..kkkkk. Cabinet reshuffle is only remedy.. Not these empty tins only making noise to Peter without facts.

  11. Mmene akuyankhulira makape amenewa zikundikaikitsa ngat zinthu zingasinthe or kuwapatsa zaka 30……anthu oipa awa adpp.,anthu omva zawo zokha…

  12. zitsiru ndizokumva zimene akunenazo chifukwa akuyankhulayo simunthu wamoyo ndimzukwa ukuyankhula,munamvapo kochi wa team ikaluza nanena kuti tachita bwino kuluza tikakonzekere bwino?za ziiiii

  13. Even mwana wa standard 1 akudziwa kuti dpp yalanika …alimi chimanga chikuwolera mnyumba mwawatsekela msika…magetsi kulibe….madzi kulibe….tsankho ….corruption….tsankho pozenga milandu …tsankho posankha mipando etc

  14. Very sorry for Dpp,its new to see apolitical party gets smiling of deaths it means,it can not help people’s problems instead they can cheers the bottles and says yes to floods,corruption e.t.c shame on this government.

  15. Very sorry for Dpp,its new to see apolitical party gets smiling of deaths it means,it can not help people’s problems instead they can cheers the bottles and says yes to floods,corruption e.t.c shame on this government.

  16. If you got no good excuse jst stay quiet..
    U won’t have words come general election..
    What a sleeping dog are you????

  17. Losing is not a blessing, and it will never be, that is mourning….
    Cry of a minister to please the big man…oh no..
    The President is surrounded by lies..

  18. This is what we call WISDOM at its best, the loss was a true blessing. Time for u guys to re-strategise. May the best party win.

  19. Kasaila shame on u. U’re speaking pa tiudzeni ngati mwabadwa kachiwiri. U’re now telling Malawian that losing by-election was a blessing in disguise. Mwadziwa liti zimenezi? Kasaila U’re one of the rudest minister/spokes person DDP has ever entertained

  20. Asadandaule a Katsaila,they only have 18 months in office,come 2019 tichotsa ndi vote anthu osamva ngat amenewa…by elections was just a starter,zenizeni ziliko 2019..Dpp yakwana ndipo yafika potithina, no vote for Dpp in 2019 ndithuuuu

  21. Mumatokonda nthawi ya zisankho zikantha basi mumaiwala pano MCP yakudzidzimutsani ndi tulo tanuto boma losadziwa kuti zinthu zikulakwika nde mukoza chani nthawi yantha muziona mbiteeeee!

  22. 😀 😀 😀 nde mmalo mosintha akupangabe zomwe zija. Tamva ku Mulhakho, mmalo mopanga za umulhakho, mulhakho became a political field kuyiwalanso kuti it was a Cultural event. Samamvetsa awa. 2019 they will get a 6 – 0 loss 😀 😀

  23. Actually I did not read the post but I think the girl has no right to beat up her boyfriend in public. Maybe they should report the matter to their village elders but if the neighbour refuse to pay his rent they should just kill the landlord and forget about the missing chicken.

  24. As long as my good APM keep holding this kind of gold-diggers who are now trying to cheat him with some new tricks, he must prepare to fall big time!

  25. DPP yaketu ndiyomweyi yomwe inatenga boma ili Ku opposition. Ngati inatenga government ili kotsutsa, nanga zikhala bwanji poti ikadali mu government! Ndizosatheka the Mighty DPP kuzaluza 2019. Am doubt.APM 2019 government basi.it was the same APM,same the mid night 6,same cabinet, same Dausi that make The mighty DPP to take government from peoples party History leapit it’s self.

    1. when you say “history repeat itself therefore MCP will rule this country for 31 years kkkkkkkkkk kuzibaya pa chifuwa

    2. Feel sorry of subjective thinking buddies like you! So you think dpp is for ever ? People are tired of this your evil dpp unless mutiuze kuti mukavota ndinu nokha ndi azibale anu?

  26. Mitengo yake ya chimanga ngati izakhale imeneyi aaaaaa ndakayika ngati muzawine for sure you don’t know how much the poor farmers are going through

    1. mtengo wa chimanga uli bwino.njala yatha.mulimenso china chimanga chaka cha mawa 2 thousand thumba and the country will cetebrate.pepa olima

  27. Akasaila,anthu musawananize,kuti inali frendly much,n’chifukwa chiyani munkalalata kuti MCP ku lowershire siyingawine? dziwani kuti amalawi tidatopa nanu ndipo 2019 we are make to change.mwatiwonetsa mbonawona and tadziwa kuti —kusadziwa mwana wambuzi adayamwa tonde..

  28. Mukumunamiza president and you advise him wrong things and mukumakhala ndi mwano mukazuzulidwa and kubakila zolakwika. I like your motto saying we are a listening government but you are stiff necked to the extent, you dictate things. You put much of your trust in chiefs, who mislead you. You are full of promises than doing it. You are ruling but you are campaigning for 2019. Just do it as Bingu first term ( ntchito zamanjaanga zindichitile umboni). Joyce magetsi she did it but inu mwakalanya. Mwachosa anthu angati ntchito kuzela vuto lamagesi. Kuba it’s worse but you point only on Joyce Bandas time. Ntchito mukapeleka legally anthu amapasana ntchito but illegal and in the end nothing on the ground. Do you remember 2015 Evan De Meya had funds for Rumphi to Nyika but you politised the whole issue. Miyala yamaziko mwayika malo angati but nothing chikuoneka. Kasaila you are just royal for your pocket but not helping the president and country( eee bwana). Mulli guards killed anthu muphiri lamulanje and instead anthu were jailed. Chipani chachuluka mijedu, anthu akuopa kulowa because of their reputation. Cadets using panga knives to threaten and injuring innocent people, just to fulfil your agendas. Up to extent of now having guns. The mess can be easily stressed but chipanicho chasanduka property.

    1. Kkkkk one kumva kukoma kuti anthu akuima poyela polongosola zakukhosi kwawo ,Inuu a DPP, anthutu asukusula sopanoo muzaone ngat ndimalawi wakale yemweuja.Tatopa ndikutipopa magazi ife iyaaaaaaa tionesana 2019 ndithu 2019 woyeeeeeeeee

  29. Kkkklkkl! Kusowa chonena a Chule a DPP.
    Pano ndithokoze Chauta chifukwa chokokola nyansi zonse (especially from MCP) zomwe zinali kuzipani zina ndikuziwunjika ku DPP.
    Izi zatipatsa mwayi a Malawi odziwirapo ntchito zanu zonyansa. Ndiye apa musati it’s a blessing but just say the truth that it is a curse. Chenjerani 2019 angelo a Chauta akubwera ndi chikolopa chodzachotsera masanzi a DPP yanuyo.

  30. And adziwe kuti njira yobera ma vote sidzatheka chifukwa anthu anachangamuka,ku opposition akudziwa kale ma plan anu odzabera komabe izo zidzavuta chifukwa M’malawi aliyense wa nzeru wadziwa chowonadi,mukuba osamangana tsono ngati mukulephera kumanga mbava yoti munayiyimitsa pa ntchito zanu zidzayenda bwanji? Apo zinadziwikiratu kuti ngakhale Peter,Gondwe ndi ena ambiri ali nawo mumgulu lakuba ndalama za Chimanga,nanga nzingati zomwe ife sitikudziwa?? Mwaononga kwakwana”NKHANGA ZAONA” dpp ulendo basi

    1. Dziko kuwawa lili lako lomwe umenewo ndiubwino ???? Wapantchito,Mulimi onse akudandaula nanga kuli bwanji wina amene akusowa ndi ntchito yomwe aakudandaula motani?? Palinso chiyembekezero kuti angasithe zinthu??? Dzana lapitalo JOSEPHY NKASA nayimba nyimbo,”KULIRA KWADZIKO” munkuyimba kwake akuti anaona wina aliyense akulira,wamalonda,mlimi,wapantchito,anthu osauka nao akubangula kwambiri. izo ndi zomwe zikuchitika panopa anthu ambiri akulira,komanso NKASA anapitliza akuti”anaona kuPhiri kumene(ku boma ko) akulira,and nthawi yao ikudza yoti alire,akukhumudwitsa wanthu,kusatumikira paudindo wawo,kumabandalama zomwe zimayendera kuthandiza wanthu mdzikomo iwo nkumaba nkumayika m’matumba mwao,nthawi ikudza Yodzasankha tirigu,namsongoli tidzamuotcha ndithu come 2019

  31. The same kasaila amati mcp ku lower shire singawine and now mmalo moti avomeleze kuti zawavuta but is coming with another tune!! I have never ever seen a stupid minister like kasaila.

  32. Ife sitikufuna pitala koma ngati INU muli kusogolonu mwakonda pitala kaya DPP Itha ngati makatani mukulambula mseu kuti MCP izaduse masavutika 2019

  33. A kasaila maloto salesana and keep on dreaming!! And mwaziwa liti kuti your party is messing our country!! 2019 you ll never win mark my word and its too late for dpp to gain people’s trust! Shame on you!!

  34. Last minutes of a dying goat! Mufune, musafune, paulendo.

Comments are closed.