Chimunthu Banda survives car crash

Advertisement
Chimunthu Banda

Former Speaker of Malawi Parliament Henry Chimunthu Banda on Friday escaped death in a car crash in Mchinji.

The car Banda was driving, a Toyota Prado, was involved in a head-on collision with another vehicle causing it to overturn several times.

Chimunthu Banda
Chimunthu’s car at the scene of the crash

Reports show that the other vehicle left its lane in a bid to overtake other cars but ended up crashing with Chimunthu’s Prado.

Chimunthu told the local media that he was fine and would seek medical help in Lilongwe.

“I thank God for he has saved my life. I feel okay but will seek medical help,” he said.

Chimunthu was on his way to his farm at Kapiri in Mchinji when the accident happened.

Advertisement

64 Comments

  1. anthu oipa awa, nduna zokhomerera zonse machende awa pamodzi ndiabwanawo.Achinyamata ife tikumavutika pamene inu mukudyerera ,nthawi yamavoti ikamafika kumangoti ine ine kunyerokwanu mumanyera zokazingirako ,mukamachita ngodzi chonchi muzitengerapo phusiro ,ndatopananu .Mukamatinamiza mulungu amaona,komaso chilango chilipari pasipompano,oipa nonse akulangeni .Chapondayu akumusiya pati? watilizauyu wokumvaamve ondifuna andiimbire pa09 ,ndatopa ndiuphawi tizingoomva zachumachanu ine phawi ndimayesesa mumatikhomerera ,ine malawi

  2. God is Great ! Chimunthu is our History in Malawi. He was handling debates with lovely commending voice with no bias mind. Kuno Kumzimba tikuti Chiuta nimuwemi pakumunthaskani Ku ngozi yikulu na yakofya! We wish you all the Best.

  3. It happens, its a secret between u and ur God, even non politicians, Christians Muslims, cadets, presidents can be involved in road accidents, It wasn’t his time to loose his life,,Chiuta watumbikike swiiii

  4. Madala Ngati Simumapemphela Kuyambila Lelo Muyambe Kupemphela Mulungu Alinanu Cholinga.Ndalezi Izi! Madala Zitayeni.Mutsateni Yesu Mwaiye Muli Chipulumutso,chitetezo Komanso Chigonjetso.

  5. or akanafa ndilibe nao vep athu andale akumalawi ntchito kuba bas mmalo mopanga chitukuko achina Dausi anayamba ndale ndikamudzu banda mpaka lero koma kumwa kulibeko chitukuko cholozeka shupit zanu inu athu andale nonse kupatula abwana lucias Banda koma ambirinu ndinu apumbwa

    1. Ngat Mmalawi Muno Muli Munthu Wina Opanda Chitukuko Ndiye Lucias Banda Ndimmoz Mwaiwo Koma Toney Ngalande Osat Manyowa Akowo Wapangako Chani Bandayo Tel Me Braz

    2. ndiwe chisilu, opusa, kupepera. ziko silimasitha ndi atsogole okha ngat malaw siotukuka you are also rensponsible mumakavotera nokha, lucius wakoyo palibe cha nzeru chomwe akuchita. chimunthu sakupanga nawo.usamale

    3. isaac iwe ndiye kaya kaya bas iweyo or utawavotera andalewo palibe chomwe ungasithe pa moyo wako mpaka uzalowa mmanda uli mphawi mmalo mot uzilimbikira ku vepa kut mwina uwone kuwala kwa ziko lapasi uli busy kusapota zipani usova fana

    4. Alipo a ndale angapo kumpanjeko sindimawaonera kukondwa anayamba ndikamudzu koma mpaka lero ali m boma koma palibe chadzeru chomwe anapangapo mudera mwao

    5. Ngakhale leronawe uthakuyambandale tionezitukukozako kkk ndkusekangat zabwno mmm. Ukumayendanjomba ngakhale akazako n anaako kulibwanj zko kapena dera?

Comments are closed.