Sindinapinyolitse chipani ine – watelo Atupele

Advertisement
Atupele Muluzi

Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF), a Atupele Muluzi ati iwo sanapinyolitse chipanichi kwa a Mutharika.

Atupele Muluzi
Atupele: Sindinapinyolitse chipani

A Muluzi amene ndi nduna mu boma la a Mutharika anauza anthu ku Ndirande kuti iwo ndi anyamata a ndale zamakono zofuna kumanga dziko.

“Zikatha zisankho, timayenera kuyamba kumanga dziko. Ine ndikugwila ntchito ndi a Mutharika kuti tithandizane kumanga dziko,” anatelo a Muluzi.

A Muluzi anati ndi ndale zachikale zomakokanakokana chifukwa choti munalikhilana mumchenga pa chisankho.

“Dziko likutsogola ndiye machitidwe athu a ndale nawo atsogole, tizigwilila ntchito limodzi,” anatelo iwo.

Pa msonkhano omwewo, a Muluzi analandila a Clement Chiwaya amene anali nduna nthawi ya a tcheya koma anapita kwa amayi.

Advertisement

154 Comments

  1. This man is dreaming, in his dream he can see UDF that one bar left. The end of ambitious. Be smart don’t make deal with croocks.

  2. munthu ofuna kukhala President sayenera kukhala munthu osintha mawanga a mayenera kukhala munthu wa nganga muchipanicho,ngati Lucius banda.

  3. Mwachita bwino ngati mwatero Mr Ndale zimafunika anthu okhwima mudzeru osangoti ndadzuka lero basi mkuyambapo ndale mmmmmm! Sichoncho ai ndipo takunyadilani. Ingoyambani bizines. Asi kaya kaunjika kaya ya msomba kaya ziwala basi

  4. CHIPANI NDI CHA L BANDA CHIMWANA CHA MULUZI DYERA BASI KODI TINDALAMA ADA ATATE ANU TIDATHA KALE.KAPHE NSOMBA KU KIA KAMUZU ADAKUMBA DAMU UPUSA DYERA BASI LUCIOUS BANDA WOYEEE .LUCIOUS

  5. Timalimba mtima kuti tidzakhala ndi president wachinyamata koma aaah ndikaona nako kalibe kulimba mtima. Komanso ntakayang’anitsitsa ndapezanso kuti nkadyera kamunthuka. Bola Lazalo kapena Petulo kkkkk

  6. Kkkkkkk koma kugwira ntchito limodzi thats great idea Atupere keep it up. Za chipani ziyike nthawi yikakwana nyamka kumakapen baxtu man ulibho enawo asakulakwisepo pano.

  7. Atupele moto kuti BUUUUUU ine ndeweniweni wa atupeleyo,nkhani yakuba ndiyina sizikugwilizana ndi atupele ayiiii kambani nkhaniyina ngati mwakhuta khobwe pitani kuchimbizi mukazithandize.ATUPELE NDI DILUUU ana mwachepa.

  8. Atupele ndiwanzeru adaionela patali pano bambo ake akunzunzika ndiye musaiwale kuti zofanana nthenga zimaulukila limodzi kuti mufufuze Atupele sakukhudzidwa ndi zosolola koma akuteteza bambo ake MCP ikalowa m’boma adzapiso komweko koma at the end chipani kutha ngati makatani.

  9. Atupele tinakuonani kuti munagulisa chipani chathu so chimozi mozi ifeso ungatigulise chipanicho apitilize kuchisogolela Lucius banda munthu osatekeseka ayi osasintha sintha mbali.

    1. Lucius ndiotchuka ndikulimba mtima komwe, koma sapanga qualify kukhala president. Pali malamulo okhuzanso maphunzilo amunthu. Ndiyesa Soldier MSCE certificate ya fake ija anamulanda nde mpomuvutilako pang’ono mpando wa upulezidentiwu kuimilila.

  10. 2024 Atupele adzakhala mtsogoleri wa dziko. Boma la lero lidacoka mu UDF. Chomwe akugwirizana anthuwa tonse sitikuzizindikira. Palibe munthu amene amafuna kukhala otsutsa ayi!! Atupele sanalakwitse kugwira nchito ndi prof ApM

  11. Ine atati ayima bambo ache Dr Bakili Bakili mluzi, atchair nditha kuzaponya voti yanga,vuto Atupere tidamkonda kwambiri poyamba koma mphamvu zautsogoleri zikuchepa, salankhula, sasusa,ayi komabe Ali booo

  12. Game hot now for Atupele thus why he’s coming out of cocoon to explain some issues that have left people speculating. Too late to save Jerusalem. It could have been pachiyambi pompaja osati lero ai. Waona chani kamchacha. Hon. Atupele, let me tell you the truth here in case Ken Ndanga gives you false hopes. You may see people flocking to your rallies but they have so many questions that need your answers. UDF will never be a national party again. Some people assume leadership positions in UDF NEC they think you have money or they’ll have contracts they’ll benefit from. Agenda for change was a good approach but has since been scorched by yourself. People out here are very furious. To convince an illiterate villager is not as simple as you may think. The language out here is that Atupele adagulitsa chipani and even if you deny that today, it’ll not convince them. You could have explained UDF plans pachiyambi pompaja osati lero. In 2004, Chakwamba of Mgwirizano coalition after seeing that he has lost elections, he quickly had a press conference in which he informed the nation on a working relationship with UDF under Bingu. With Atupele, it was contrary. Quiet! Now people are about to teach UDF a lesson. Believe me, they’ll.

  13. Mungonena kwachema mgwilizano unali wa awili eni chipani sanakufune ndimaplani mumapanga ndi mpanda mano, waona kuti palibe chake ,kuthandiza chitukuko boma siungachite kulowa mkati Mpanda mano adanenetsa msonkhano waku Mangochi uja kuti kwatsala kukhazika Mbendera imodzi , Blue Yellow kwavutako mongotero kwavuta kukupasilani boma

  14. pumbwa uyu sangadzatsogolere dziko ayi Kusamva komwe ankapanga bambo ake ndinkona anawalanda dziko anzao omwe poyamba ankaoneka ngati ogotomala aka

  15. Ife tipitiriza kumukonda ATUPERE sitingavere inu a MCP mwanya nawo powona kuti ATUPERE akugwira ntchito ndi boma mwauoponda ATUPERE sangagwire ntchito ndi mcp

    1. kkkkk Atupele akukupwetekani kumene inu a kongelesi munya akugwira ntchito ndiboma kuphunzira kayendetsedwe ka boma mawa tikamutsankha kukhala president sadzavutika

    2. Kkkkkkkk!! Ndikukaika ngati a MCP angafune Atupele,coz sangakwanitse kusintha zinthu.Its shameful to see Atupele working with a failing gvt of Proffesor,Kkkkkkkk!! Atupele is not a brave politician to say no wherever it is needed

  16. KKKKKKKK OKAY BAMBO ATUPELE MULUZI, KOMABE musaiwale KUTI simukulankhula ndi Ana & nsonkhanowo mumapanga masana sikuti unali usiku, Nde musakhale ngati mukuuza ana anu

  17. Koma tikumbuka kuti ma sapota a UDF ndi DPP adayamba kukangana ku Mangochi zotsatira za chisankho zisadathe kuulutsa? Kodi UDF ikadakana kugwira ntchito ndi boma, dzikoli tikanakhala pa mtendere chonchi? Izi ndiye ndale zoti tiphunzitse aMalawi. Ndale zokhobolana zija ndiye zidatichedwetsa chitukuko.

  18. Anthu Opusa Munapanga Bwanji Ndinanena Kuti Nkansa Ndimupasa Galimoto Ineeee!! NDINANENA KUTI Nyimbo Za Mkansa Zimakoma Kumvela Mugalimotooooo!!! Amufoilisa. Ndimadolo Yawa Samalani

  19. Ndale zaku Malawi zadyela basi ngati akaphathikana ndi chipani cholamula iye pamene ali otsutsa akaona cholakwika akwanitsa bwanji kutsutsa? Ndale Atupele wachepa nazo sangakwanitse kutilamulila ameneyi.

  20. Atupele what you are doing in my view may be construed to be politics of selfishness. Where kugwira ntchito nfi boma only mean you and indee you alone must be a cabinet minister. How would you let the contribution of others in UDF count too?

  21. You learn through mistakes….. Zanus izo baipisani mbili yadziko lanthu labwinoli mbuzi za anthu inu muuzane mitu kukula ng@ nyumba yopanda plan…

  22. NDALE za ku Malawi, dziko la anthu osamvetsetseka. 2014 kunali ukulu ukulu ndi ungono ungono. Anthu anavotera ukulu ukulu. Lero Atupele akuthandiza ukulu ukulu, ndi izi mukuti akulakwitsa ,kodi iyeyu kuti akhale okhoza atani? Manyasa tell him. Atani?

  23. NDIZOWONA SANAPINYOLITSE CHIPANI AI, MAU AMENEWA AMATULUKA KUKAMWA KONUNKHA KOSACHAPA NDI MSWACHI. AKUTI IWOWO NGATI ANADANA NDI CHIPANI CHOLAMULA NDIYE NAYE MTSOGOLELI WA UDF NAYE ADANE NACHO MAGANIZO OPUSA KWAMBILI. NGATI MWAGONJA PA CHISANKHO KUMAVOMELEZA KUGONJA NDIKULITHANDIZA BOMA LAWINALO PODIKILA ZAKA ZINA 5, MULIKIILE DZIKO NGATI MUNACHITA LOBWELEKA BWANJI?? A CHEIR ANANENAPO MAU AKUTI AMALAWI TAKWELA BOAT LIMODZI TIKACHITA MA VUVU TOSE TIMILA NDIYE ANDALE AKUMALAWI AMACHITA NGATI DZIKO LA MALAWI NDILOBWELEKA.

  24. ONYOZA NYOZANI KOMA INE NDALE ZA ATUPELE ZIMANDIGWIRA MTIMA NDIPO ENANU MUTAPHUDZIRA NDALE ZA ATUPELE MALAWI AKHODZA KUKHALA PABWINO

  25. Chipani cha UDF sichayinu nokha baba mwasata ndalama kuwasiya okusatilani pa mbalambanda dyela bansi tangosiyani udindowo ife tisankha wina sitinakusankhileni kuti timakuwopani ayi kapena ndalama ayinso komatimaganiza kuti mutinthandiza koma ayi

  26. Vomelezani a Muluzi, you weakened the party single handedly, it is no longer the same UDF we used to know, it was sold to the highest bidder (DPP) long time ago no wonder it’s not even an official opposition in parly.

  27. tapanganiza nzeru zioneke maasewela basi ife tatopa ndi zpusa bamboo ako sanapange zimene iwe ukuchitaazi ganizaa bwino

  28. Atsogoleri ofuna kumanga dziko adzitero adzilekanitsa nthawi yopanga ndale ndi yomanga dziko 2024 Atupele muluzi ndi boma basi udekhe after moya ndj iwe basi zikumunyasa adzilume kunsana

    1. mumafuna Atupele adzipanga zombwambwana nga chakwera?ufumu umapita kwa anthu okhawo odekha ndi odzichepetsa Atupele 2024 bomaaaaaaaaaaaaaaaa! !!!!!!!!

    2. Pasadi Katole umaganiza wava? ndale zanji zosavomeleza mukaluza makatumba wali-wali ngati mukulamula ndinu bwanji? what kind of people are you? first mcp fulishes.

    3. Ngati chakwera adanyoza mulungu pothawa ntchito yake( yona) kuli bwanji anthu ife,ng’ona zija sizibwerara? Yemwe anaona ntchito za MCP pamene imkalanga anthu sangabwererenso asinthe chipanicho dzina mwina tizavola ichocho.Koma MCP mmmmm

    4. Musaiwale Anthu Aja Anafa Pazioneselo 2011 Aja,pamalaw Palibe Chipan Chabwino.Tien Tingosankha Yesu Samakhumudwisaamapasa Mtendele Wamumtima

    5. Atupele anagulitsa chipani ku dpp phindu lake amalipeza ndi iyeyo ndi bambo ake
      Akuteteza bambo ake kuti asakwidzingidwe paja nawonso ndi tsizinantole
      Phindu lenileni kwa munthu waku mudzi palibepo

    6. amalaw chot mudziwe chakwela sangawine upresident adathawa ntchto yamulungu kutsata za dziko kumalankhula zosemphana ndi mau amulungu ameneyu mulungu anakwiya naye thats y sizikumuyendela

  29. Timawaona ngati ali ndi mzeru monga wachinyamata koma mmmm alibe mzeru ndi adyera, ozikonda apereka chipani chikulukulu ndithu

  30. Kuteteza mbala ija idaba ndalama za boma zokwana K1.7 billion. He has disappointed 900000 people who voted for him, 2019 adzamuvotere ndi makolo ndi abale ake basi, munthu wadyera, ine abweze voti yanga bakha ameneyu.

    1. Atupere ndikatundu omanga ndi mawaya _Adakalhala kuti ndiwawamba aaaaa sibwezi anthu akulimbana naye ndiyetu simunati chifukwa ayamba kutikita iweyo amene ukudzinamizawe kuti ungakaime ndi Hon Atupere ku convetion we ndipo ukagwa mochititsa manyazi chifukwa mavoti ako ndi 34 kenaka tikamalizirakulu wako amene akumakupatsa ma tshirt ankhuku pasanayo ndi pamene mudzamudziwe Atupere mumangomuona kufatsa etiiii

    2. Mbuli ndiimene sikudziwa kapena kuvomeleza kuti Bakili Muluzi adaba ndalama za boma, ngakhale mwana wa ku primary akhoza kukupambanani kuzitsata zinthu. Koma umbulidi ndi matenda ndithu.

    1. Choka what is wrong with achawa it’s this topic about chawa people muli ndi bvuto bambo inu why do you hate chawa so much?

  31. UDF yatha ngati makatani, a chair woyeeeeeeeeeeeee!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!

Comments are closed.