Kongeresi inazolowela kuluza ndipo 2019 tiyitibulanso – watelo Mutharika

Advertisement
President Mutharika

Mtsogoleri wa dziko lino amenenso ndi mtsogoleri wa chipani cholamula cha Democratic Progressive (DPP) wati chipani chotsutsa cha Kongeresi chinazolowela kugonja pa chisankho.

Mutharika ananena izi ku nyumba ya boma mu mzinda wa Lilongwe pamene chipani chake chinakonza mgonero.

President Mutharika
Mutharika: Kongeresi tiyitibulanso 2019

A Mutharika polankhula kwa otsatira chipani chawo ananena kuti iwo ndi chipani chawo apambananso chisankho cha 2019.

“Ikafika 2019, wina asakunamizeni iyayi, tikupambana chisankho,” anatelo a Mutharika.

Iwo anati chipani chawo chilimbika ndi kuchita kampeni mwa khama ndipo pamapeto pake azapambana.

“A Kongeresi musawaope, aja ndi olephela basi. Chimene amadziwa ndi kulila kuti abeledwa chisankho. Alilanso 2019.”

“Paja 1999 analira kuti abeledwa. 2004 analilanso. 2009 chimodzi-modzi. 2014 analilanso, muwaona 2019 akulilanso kuti abeledwa,” anatelo a Mutharika.

Advertisement

226 Comments

  1. maliro amapepuka akakhala kukhomo lina koma akafika nyumba mwanu pomwe mumaona kuipa kwa ifa.mau omwe akuyakhula iwowa ali bwino kwaiwo poti ali boma koma akazaluza mau omwewa azasandulika woipa kwaiwo ili ndidziko zithu zimasitha amadziwa ndani kuti iwowa nkukhala mtsogoleri wa dziko

  2. You lie Muthalika this time people will not vote for parties,will vote for someone who can bring hope to malawi nation,,this time malawi is a wokeup nation they know how you have mangled and crippled Malawi to wheelchair,malawi is nothing now bcoz you,,,careful! Don’t talk about MCP first look at the mess you’re doing there

  3. Olo atandithira doom mkamwa, sindingavotere kongeresi,, mcp,, UFITI CHANI???,
    SINTHANI DZINA LACHIPANI KUNO KUMMWERA OVOTERA KONGERESI AMATENGEDWA NGATI ALI NDI UFITI KKKKKKK

  4. Awa Siwofunika Kulamulira Dziko Ndiwaphokoso Osati Chitukuko. In This His Term Tivutika Guyz Munthu Uyu Adazolowela Ku Amerika

  5. Malo Mothetsa Umphawi Mukulimbana Ndiife A Mcp , Kod Zinthu Zimene Mukugwiritsa Ntchito Adapanga Ndani? Miseu, Milatho, Maofesi Aboma, Air Pot Etc. Mbuli Iyi Late Bingu Adali Wachitukuko Osat Izi Ati Okuti Ndiwasukulu Aaa Kaya , Akuchita Matha Ndi Mcp Kapeyu Pano Ndalama Odatsekela Ku Bank Ndi School Yawoyi. Mcp Boma 2019!!

  6. moti akonze .mavuto ali ndziko muno busy kulimbana ndi mcp basi zinthu zikudula ndalama / ntchito kusowa zipangizo za ulimi kukwela mtengo koma mbewu muli akalima kumakagulitsa motchipa pali mzelu apa musamapange zomatitosa dala cholinga tidzitukwa stpd!

  7. Kodi Ndi Manfesto Amene Mudatiuza Ngati Ayi Mukananena poyamba Kut Ndizalimbana Ndi Mcp Ndikazawina Sikanakuvotelani Nenani Zveka Osati Kunyoza Azako Ayi.

  8. kodi mbuli zalomwe mukuti mcp idzalowela kuluza, kodi dpp isanalowe m’boma poyamba amalamula ndani? Muzithokoza mulungu chifukwa kamuzu adalindimoyo wawumunthu adakakhala ndimoyo ngati mugabe sibwezi akatangalenu mukulamula. Timavota ndife tilindiwufulu kuchotsa wava chigendele chamlomwe.

  9. 85 year of age koma akuti ayimaso pampando yet mumati achinyamata ndi atsogoleni amawa,, mawa lake liti?? zimandiwawa kwambiri!! wabkhura mopusa Pitala

  10. M c p will never rule until this generation gone believe me there is no any Dolo in that party D p p is full of dolois wake up and see far

  11. adzawina pot adavota kale ukhala ufumu wakumwamba bwez tasilila kma wapadziko aaa mzotsala zmenezo monga mmene amakhali mulundo wapanyumba yamunthu mwini nyumbayo akamupanga trasfa samutenga amamsiya

  12. if you are failing to run government we better join tanzania or zambia as one country.
    ingokhala south tanzania.

  13. Ndiye chikuwavuta ndi chiyani a president panopa tikungomva za MCP mmalo mowaudaza anthu mmene athanire ndi maviuto akuta Malawi panowa

  14. Boring President Malawi Eve had, bring development to the people not fighting with opposition.. Majority of Malawians are really tired with this idiot.

  15. M’malo mokoza njira zotukulira dziko la malawi muli bizy kulimbana ndichipani chotsutsa pali nzeru pamenepo i thnk ur going mad mr man blaz mericano mulomwe iwe

  16. Khokhokho!awuzen man phiko,ndipo 2019akulimbanilanayo kodi sakudziwa kuti munawina kale opanda opikitsana naye, PHIKO 2019 BOMA ILOOO!!!

  17. Apeter mmmmmmmm………. Madzi anu anaola see 100% 90% for McP and 10% for dpp mudzayeseleso Ku bera tidzaona gati Ndi ma bodgard akowo sakakuukila mwatikwana Ndi bodza myapapi iwe

  18. Sidaziwone Adacezela Kuziwona Dikilani Pang;ono Adpp Muziwona Moti Inu Adpp Mukuganiza Kuti Amalawi Akusangalala Nawo Ulamulilo Wanuwu? M Malawi Wozindikila Sangavoteleso Dpp Koma Yekhayo Amene Mutu Wake Nsukuyenda Bwino

  19. Zafodya zimenezo, uwawuze a MBC azikuonesa zomwe adpp akuchita Ku msonkhano was MCP? Akumalowa chipani chimwecho chikunenedwacho

  20. A Tcheya ananena kale kuti ndani sakuziwa nkhanza za kokoliko ife tikupita chitsogolo osati kubwerela m’mbuyo this country is moving followard 2019 maso pa Blue colour

  21. Mwitha Emanuel don’t you see that your president is afraid of Chakwera? there is AFORD, PP,NASAF, jst to mention few political parties, so why targetting MCP only? akuopa Chakwera MCP 2019 bomaaaaaaa!

  22. Kodi peter yo amaona ngati anthu aja amabwera kuzamva fundo zake? Anazindikramochedwa anthu kuti amene uja amangopanga ma jokes basi. 2019 chakwera basi

  23. Palibe cha phindu amakamba pa nsonkhano,ntchito kunyoza congeresi,ma donors,ma NG0s eish or ayale mwala wa madziko or kukweza ufumu.Dziko silingatukuke nd zimenezi

  24. ndpo ine nkuvomeleza coz palibemalo atambala wakuda boma kod mukufuna pta apangechan kula mulilaziko sikofewa munthu akupanga kaye zamsewu them

  25. Ndikanakonda muziima pasanja kuwakumbutasa anthu zitukuko zomwe mwapanga chifukwa anthu akuona okha osawapangira zochita, Ikakhala voti tikasankha maligna ndintchito zachipani osati chifukwa choto auje ndikwadziwa ayi.

  26. IWEYO UKULAMULILAWE UKAMATI UDZAPAMBANA MU 2019, UYIWALE! CHIKUKULANKHULITSACHO NDI CHAMBA CHIMENE UMAMWACHO ZIMENENZO UZIUNZA AMAKO!! KUBELA MA VOTI SI DIRU, NDICHIFUKWA CHAKE ZAKUM’VUTA! TULIRATU PANSI UDINDOWO IWEYO USANATHUDZUKE CHIFU.

  27. Mr presdent or wateva they call u..
    Let success fight for u kulimbana ndi.opposition kukubwereserani nthenda yachirendi ya kadya nka Gert

  28. shameful president, he don’t have ideas of how to run the country, hence fighting opposition, your days of staying in palice are numbered. Ufumuwu ukuperekedwa kwa ena Mwakanika baba.

  29. koma agalu inu uciclu,umbli pa chizungu kugodomala,kudontha ndi uchidempete,ukulemerani/ukukhwephani kumangoti kubera! kubera! inu mudali kuti? where were u? a MEC nkuti asadabadwe? mbuli sipeza mpata apa ingaononge sha!! Dpp 2019 boma!!!

    1. mbuzi!
      iwe kanyimbi wamunthu.pajadi anthu akummwera mukaphunzira kwambiri mumasiyira standad 4 eti?
      mackson mbendera alikuti?
      simunamuphetsa ndinu ndichisoni mutamulumbiritsa mokakamiza chosecho mwabera?
      muzithokoza omwe adakuthandizani poberawo kuti adakuchotsani umphwawi.
      mpoti mudyeretu.mbava zawanthu ngati inu.

    2. what about u, if i’m kanymbi? he? am not CDSS student wava? ngati ukufuna lira kma Dpp 2019 boma!!! ngati chikulira tachionani.

    3. what about u, if i’m kanymbi? he? am not CDSS student wava? ngati ukufuna lira kma Dpp 2019 boma!!! ngati chikulira tachionani.

  30. Ndipo bige zomwe mwathyakulazo ndi zoona congiresi inazilowela kuluza mzosatheka kuti angakalowenso m’boma, boma lake liti Malawi? aaaa anthufetu sitinaiwale nkhanza za congiresi tabwezedwapo Ife Ku school, nkhani take khadi, aaaa iyai abapuma nthawi sinati

    1. komadi ase sukunama kumwera kuno ndife anthu ovetsa chisoni kwambiri tidasiyana ndi anthu a chigawo cha pakati ndi kumpoto amava chifukwa cha fundu za munthu osati kumwe munthu akuchoka,vuto kuno ndi school

    2. Apresdent mmalo motuuza mfundo zomanga dziko inu muli busy kutifotokozera za otsutsa,,,,,, Tinakusankhani tokha tidzakuchotsaniso tokha ndiye chonde musathe mau chifukwa mpandowo ndiosiilana…..

  31. The real government never worst its time with opposition…fight corruption and poverty bwana President tikudalira inu dzilemekezeni….titukule dzikoli….otherwise this time ndayang,anna maso ku Tambala wakuda Dr Chakwera my Final hope!!!! osati Chona wamantha Pitala

  32. kkkkk akuona kuti adzabelanso eti sizaulendo uno moti aziuzilatu asilikali ndi apolice kukozeka kupha athu chifukwa zitidzaiva olo pang’ono pomwe iwe ukusiya udindo pansi team mcp

    1. @willard u will weep ma dia friend Malawias hv oped there ayez they no longer sleeping there will be no such hacking information anymore we are watching with interest otherwise u will nt belive whn the real winner will be announced with ought the electrol chief crying kkkkk mark ma word

  33. Says the president who fails to fix shit pipes in lilongwe,pipo are drinking unclean water and u have power to stand up n talk shit to opposition!maaaaaad!

  34. Iwe Jimmy ovota ulipo wekha ? Or mbumba yakwanu itati isavote kuphatikiza ndi ambwiyako omwe ukuganiza kuti Amuthalika sangawine ? Uzinena zoti a2 akumve bwinobwino sizotinunkhisa mkamwa apa tiye ukooo ! Kkkkkkkkkkkkkkkkkk Mmaso mwako wamva iwe mbuzi .

  35. Azachita kubela ndani akuchifuna chipani cha anthu okutha mkamwa mano, akuba ngati amenewa. Akafunse anzawo ankadzitcha ati mtunda wina pano mtundawo unatha anthu anausandusa madimba akulima mpiru ndi tomato, chipan chawo anachipinyurisa ndi mulandu wa ndalama za 1.4 billion

  36. Dont fight MCP fight poverty, unemployment ,inflation,nepotism,good salaries ,workers rights etc oppossition parties are your development partners remember government is made up three arms . Work together

    1. the opposition don’t want to work together…ur arguments unemployment,poverty and the like exist even in the US.Its time for malawians to be smart and avoid dependency

    2. Christopher Ndovie what you see on the papers is not what actually happens on the ground . check with parliament as to how many trips have the members of the opposition made this year representing Malawi govt. They always work together only that at times they differ in policies . And even the countries you have mentioned their battle is against poverty. Making America again will not happen by winning against democrats but by making sure the basics are provided.

    3. on point @ inkosi don’t fight MCP fight against poverty,unemployement osati kumatiwuza zausilu ife tired with trash he is a big failure

    4. Bertha Hawells Beza…u should also wake up and smell that coffee urself all am saying is unemployment is a problem everywhere.we waste our time with the gvmt instead of finding ways on how to survive ourselves

    5. @chris the word gvnmt means pipo and in za its nt all pipo can rule we chose then those who are chosen and opposition must find solution as u hv said we must find solution hv u ever go to the bank asking loan to start business and wht thingz they want thats the job of the ruling to soften them if u said even America got no jobs bt find hw many percent do americans hv compared to us be serious as gvnmt they hv failed the youth the eldery yap we dont want them to do 100percent bt try avoid chaponda system

    6. Mwayi Masah Banda a president ananena kuti mdani wawo ndi zimene ndatchulazi pa convention mu manifesto komanso mmisonkhano yoyamba now party politics ikumusokoneza ma dreams amene anali nawo poyamba

    7. A dpp apangako mbaliyao nanga inu a mcp mwapanga chan kupatulapo zomwe anapanga Kamuzu?.Munamva kut chipan chikakhala chosutsa ndye kut sichithandza pazitukuko?mukudikila kulowa m’boma kae? kkk ndye liti pot 2019 dpp ikuwinanso musunge mau angawa muzawakumbuka #Peter atawinanso mukhalira yomweyo yomangolotayo

    8. midoli yomwe mukumwa a dpp dziwani kuti ikubwererani posachedwapa.mufa ndi agogo anuwo ndipo asowa okuponyerani nthano. ziri ndi aeni ake izi. mia,chakwera ndi msowoya sakukugonesani tulo dziko likudziwa.dpp yonse munthu wopanda mbiri yoyipa mkukhala chilima yekha? zamanyazi.

    9. Kkkkkk but how much is a bag of fertilizer? For ur on information most of pipo here in malawi they depend on their harvested yields to buy fertilizer and the like so if u estimate urself how many bags of maize can a farmer sell just to access one bag of fertilizer?.i surely tel u most pipo will not cultivate if that nonsense k4000 will continue which will result in famine

    10. @phiri Good…not even if the banks are softened up,u cannot just wake up and get a loan from the banks not even in the countries where they are financially stable.its a lose game to keep on talking about the govt rather individually start developing skills of survival urself coz if u dont in the end ur the one to suffer.

  37. Paja Goliath naye a mkatelo pomunyoza David !!! Let’s wait til the time but plz don’t bring the past remember time changes. Moreover u knw nothing about tomorrow so for now zip up yo mouth

  38. Akunena zowona xi boza ai mcp singawine inu aaaaaa. Mmafuna azinena boza???????????????????????????? Mcp iwala zowina. Dpp moto kuti buuuuuuuuuuuuuuuu!!!!!!!

    1. aaaa..ka vote kako tidzangoponyapo ma vote 1000.. kkkkkk..sikadzaphula kanthu ataaa..kkkkkk..hi hi hi hi hii….kkkkkk

  39. Nkhani kumangobweleza imodzi modzi imeneyi ndiyo iti kodi? Admin wa tsamba ili ndi kape kwabasi ndale zikutanthauzira chani?

Comments are closed.