If I join DPP, Bingu will resurrect – Kabwila

Advertisement
Jessie Kabwila

Outspoken lawmaker for Salima North West constituency Jessie Kabwila has said late President Bingu wa Mutharika would resurrect if she joined the ruling Democratic Progressive Party (DPP).

The remarks follow reports that Kabwila is on the move to join DPP due to internal wrangles in the Malawi Congress Party (MCP).

Jessie Kabwila
Kabwila: Bingu will resurrect

Further reports revealed that Kabwila got money from the ruling party to spearhead calls for MCP to hold an early convention.

But Kabwila has downplayed the reports arguing the academic freedom saga created a cat and rat relation between her and DPP.

“Inetu ngati ndingadzuke lero ndikunena kuti ndifuna kulowa DPP, ndithu kumanda kusekuka, Bingu achita kubweleranso kuti nde masewera amenewo (If I can just wake up today and announce that I want to join DPP, am telling you Bingu can resurrect to stop me from joining),” said Kabwila.

She further added that DPP cannot buy her arguing she gets whatever she wants by working and getting paid as a Member of Parliament.

Kabwila is well known for her strong stance in defence of section 33 that provide freedom of academic after former Inspector General (IG) of Police Peter Mukhito had summoned Chancellor College based lecturer Blessings Chinsinga over an example he gave in class.

She together with other academicians demanded Mukhito to apologize for violating section 33 of the constitution but the late president Bingu came in defence of the then IG arguing “A Mukhito sapepesa” (Mukhito will not apologize).

Advertisement

209 Comments

  1. Oasapanga ndale chifukwa cho mtsogoleri akuchokera kwanu, chilungamo enanu mukuchiziwa kut mtsogoleri wabwino ndi chakwera komaso osasankha mtsogoleri chifkw cha ndalama zake, dziko salamulira ndi ndalama zake koma misonkho ija! Nde tidzikonda atsogoleri anzeru pa misonkhoyo not mbava. DPP ngati idawina mwachilungamo ndichifukwa choti anthu amkayesa ngati aona nzeru za bingu koma pali mbola coz nthawi inayake abingu zinthu za ma shopo zinayendapo bwino komaso alimi ananjaya ndithu komaso zomangamanga zinalipo koma osati zalero zongomanga basi kaya nde stionda coz kudula katundu too much

  2. Kodi Jessie Wabwila chani? Mayankhulidwe amenewa ndiye ati? Mukulephela kumvana ndi amoyo anzanu ku MCP ndiye lero mwati muphwekele Okufa? Machitidwe anu akuonetsa kuti mukudziwa ndithu kuti MCP siyabwino munangolowela chipyela mtima..! May the good Lord forgive Jessie Kabwila..! R .i. P Prof. Bingu Chitsime Chakuya Wa Mutharika

  3. where ever she can go I have no problem with her Coz as much as iknow her she is not a game changer but atrouble maker,she is like Sulumba (the Nyasa Big Bullets player) wongotchuka koma wosathandiza team

  4. Tiyeni tikamakamba nkhani tisamanene za munthu amene anamwalira chifukwa mudzalandira matembelero.Mai Kabwila ziwani ichi Bingu anamwalira koma inuyo mudzamwalira liti?Osamatsewera ndi imfa inuyo sindinu munthu opambana pa dziko lapansi pangani ubale ndi Mulungu kuti mumphunzire kunena zachilungamo.

  5. No need for her to join DPP…..even Chakwela doesn’t need her….she is a prostitute. …and Chakwela doesn’t entertain prostitutes likewise DPP.

  6. to hell wt all politians,,
    its bcoz of such pple that Mw is unable to develop since 1963 to date. tiyambitse gulu la zigawenga kut Mw adzuke & selfish greedy leaders shud fear de power in pple nt us fearing pple in powr.

  7. chenjezo langa kwa kabwila nali: ukakhara usamathe mau chifukwa umdzachita manyazi mawa lino . adalipo anzako m dziko muno omwe adanyoza dpp koma lero tidawalandira ku dpp .komanso kumakamba za bingu munthu oti adamwalira kale sibwino ,

  8. DPP won election in 2009 and 2014 without Kabwila. I don’t think that she has anything important. DPP is stronger than ever.

  9. Just a mistake.she would have said, ‘…..chakwera will resurrect’,because chakwera is dead in mind.He will realise how strong DPP is after loosing alot of supporters.Its when he will start to play a true polical movie.

  10. Very certain coz he knew MCP to be a killer Party & one automatically becomes another just by that thought of being a member of the MCP.

  11. Let her do wat on her mind she is not a kid she knows wat she is doing by the way am not believe that she can join this thief party

  12. Anthu azakhala akutchulabe bingu as Tate wadziko lino. DPP still goes on nanji mavote atheka kale or itapanda kusachita campaign

  13. Zipani zonse zili ndi zofooka zake monga. Robert chasowa njaunju komaso pa 20 July osaiwala

  14. Ameneyutu kungolowa Dpp ndiye kuti tsogolo lake lokapezeka ku nyumba ya malamuro lathela pompo coz Salima maka maka dela lomwe amaimila iyeyu chiyambileni cha zipani zambili phungu wa chipani china sadawineko amangopambana ndi wa Mcp basi chimodzi modziso Salima north ndiye akudziwaso iyeyo pomwe alipo

  15. Mwayamba kare, mwayamba kare =kunjenjemera!!!! Atangova Mia walowa mcp kunjenjemera….2019 mcp basi tizizagulako zinthu zamitengo yabwino pamodzi ndi zomangamanga osati zanu mzokhalira kumanga basi mukuona ngati tizikhuta zimenenezo? Inu mutadya zabwinozabwino koma anzanu chinsima tsku lonse kaamba kwakudula kwa zakudya zoonjezera koma chosecho materials ake ndi aku malawi.

  16. This woman is now becoming a nuisance. I used to respect her but she is a re ability to MCP.
    She better join DPP even if Bingu resurrects we do not care.

  17. have respect for the dead.Bingu died we can now remember for those good things he did while he was alive…like many others Bingu had errored but that is wrong for a role model to say.

  18. Kabwira is another party herself.
    Get to know who Kabwira is.
    Evil is in her
    Not her in evil.

    Same to these other politician.
    While some are in evil
    Some, evil is in them

  19. Kkkkkkkk tell Them.Jessie ndipo azaukira mu state house momwemo kupangisa fans yonse ng’ondooooo kklk koma mathawidwewo angaseketsetu imagine Peter akulimbirana pakhomo ndi mabody guard hahaha koma movie ingKome iyi..plz Jessie try it aaa i wanna see

    1. Some people r just men by name hahaha even the bible says akufa sadziwa kanthu bii nduchimo ukupangitsani kulephera kutchula akufa..ndipo ineso ndiyankhula ngati Jersy ine kuvotera dpp bambo anga azauka kumanda….sometimes be men who understand what other things mean jersy was trying to say she cant do that equally as the dead cant resurrect ….think beyond ur nose men hiyaaa

    1. Yes my sister caro ,Malawian politicians are all the same .First they have to enrich themselves ,They all dream of sending their children to UK/US for studies .Trust me these are the biggest crooks in the world .Every politician will say what Hon Kabwira has said

    2. Tchaka ,anthuwa amangofunamo ndalama mu ndalemu .Osamanamizidwa kuti akufuna athandize osauka .Zitheka bwanj MP wa ku Rumphi kumakhala ku Blantyre ,nde mavuto a anthu a mu constituence mwake awaona bwanj

  20. The statement by honourable J. Kabwira if it is true then I find it absurd. It is not even different from that of Jeffry wa Jeffry. Politics is a game of certainties. You cannot rule out possibilities. After all, Kabwira has friends in DPP. They meet in women caucasses and forums. Bingu is gone. And gone for ever. And Kabwira cannot afford to harbour hate of that degree. We shall surely laugh at her when the opposite turns true.

    1. That’s kind of baby thinking do u think there is nothing that the government is doing Kkkk Malawi at its best politics is a dirty game indeed

    2. Reporting of such kind is not wrong. Citizens should know what these politians are saying wherever they are holding their rallies. Now media are our eyes and ears who let us know what they have seen and heard. Then we digest the matter at hand and make a conclusion what to do next.

    3. How can we develop? We have diverted focus from our daily trade to political journalism . Can’t we discuss something important? All I hear is mutharika this mutharika that , Mia this Chakwera that . We will be poor for decades to come . Just join politics if u want

    4. Be quite guys all you have to know is that politics make news as well as promince people and proximity you are Malawians so these are kind of stoties we have to hear for us to make proper ideas when voting……

    5. Be quite guys all you have to know is that politics make news as well as promince people and proximity you are Malawians so these are kind of stoties we have to hear for us to make proper ideas when voting……

    1. Mr Magongwa,i think you Don’t understand politics.When we say politics we mean all dirty things happened in our society every day.Look at Kamuzu times,Bakili Muluzi,Bingu,Joice Banda.people were killed without mercy so what do you want to say here my friend?Pandale palibe oyera ngati mwabadwa dzulo you can say That.Mind you bro don’t ever trust apolitician.

    2. Kabwila akudziwa pomwe alipo kuti kungolowa Dpp ndiye kuti wasiyana nayo nyumba ya malamuro coz komwe amaimila iye uja ku salima momwe zidayambila zipani zambiri mdziko muno sadapambanepo phungu wa chipani china akudziwaso iyeyo chimodzi modziso ku Salima north wachipani china sadapambanepo ndiye mwachidule ndinganene kuti zili ndi iyeyo bola salima akuidziwa kuti imadana ndi chipani cha anthu akuba

    3. mr kalibu i can agree with u mbuz zinaz zmangokamba za mkutu akuona ngat kabwila angalowe chpan cha kubacho ng’oo mwauponda

    4. I wonder why sometimes ppo crazy like this why Insulting eachother fo nonsese things anuwake ali pheee kudya zonona inu mukuvutika makomo mwanumo mkumawaikira kumbuyo anthu opanda pabwino ngat amenewa fuckoff

    5. Chisankha chili ndi mwini wake amene akuyendetsa Boma si anthu aku Salima okha komanso Chipani cha MCP sichili ku salima kokha ayi dziwani zimenezo

    6. who is kabwira? which kabwira? malawians very fun inded….. if call others satanists is kabwira holly? stop rwreckless remarks

  21. Please Kabwila don’t do that , we love you at MCP because of your heart of patriotic heart you have to MCP

  22. iwe kabwira iwenso galu eti? osamasewera ndi anthu akufa nyani iwe. bwanji osatchula ambwiyako anafa kalekale aja? leave our Bingu alone.

Comments are closed.