Monkeys destroying cassava tubers in Nkhotakota

Advertisement

Cassava farmers in Nkhotakota are worried of low harvests due to monkeys that are invading their farms to destroy tubers.

Malawi24 caught up with some farmers in the district who said the situation may lead to hunger.

In an interview with this publication, one of the farmers Latifa Chisisili said the situation is worrisome since cassava is their staple food.

“The situation is really bad since monkeys in large numbers are invading our farms. They are destroying both fresh and dried tubers.

“Here in rural Nkhotakota we rely on cassava for our survival since maize doesn’t perform well due to environment,” she told Malawi24.

She added that currently some farmers are spending daytime in their fields to chase away the monkeys.

Nkhotakota district is one of the districts in Malawi that takes cassava as staple food.

The problem is serious in villages of Mbalame, Chizili, Chamba, Thandaza and Nkhandwe which are under Traditional Authority Malengachanzi in the district.

Advertisement

156 Comments

    1. Anthu adakalowa malo a nyani popanda chiloledzo. China chilichpnse cholimidwa pa mthaka yawo ndi chawo. Umbombo bwanji,mtima psafuna kugawana.

  1. ndiyeno bwanji wosamanga ameneyu komandi kanakhalayine zaka zitatu ndilikundende nanuso mukasowa nghani muzingokala ndikumacheza ndibanjalanu kusowazonena mufuna mutiyanghulise pambali zawucsilu

  2. Verani izi, zomwe mungapange kuti vutoli lithe .mugwire nyani mmozi ndiye mu mpake penti ya Red thupi lose ndiye mu msiye ,ndiye akamasatira anzake aja azimuthawi basi ndiye kuti dera limenelo achokapo basi mukatero mwaitha

  3. What is the Department of Parks and Wildlife doing about this issue? If it is like the situation at my village then the answer is nothing at all, even though Regional Headquarters is only 8 kilometres away.

    1. This has nothing to do with climate change. It is because there are plenty of crops being grown for people that there is no need for the monkeys to search for food in the forests. Why should they bother when it is far easier to steal food from the villagers. As we continue to do nothing about these vermin then their numbers just keep increasing, and the new ones see that there is no need to bugger about all day searching amongst the trees when there is food just waiting for them in the villages.

    1. Choka mulomwe iwe, udzapite Ku Nkhotakota sudzapeza amasikini openga ngati mwadzadzila mmataunimu, Chambacho China mule gets an I inuyo anthu opanda malo,Nyani ndi nyama ya mbuzi kwa inu

  4. oh kk you see ..this humans they ‘re worried about us ..they say we’re the distroying their staple food …….let us eat also is our food too …
    monkeys

  5. Munawononga nkharango yomwe amkapezamo zakudya popanga minda.These are some of the deforestation results coz anyaniwa nawo ali ndi ufulu

  6. Ndiye ngati mukuona kuti akupanga zolakwika muziwapatsa zakudyazo akapitilizabe agwire ntchito yakalavula gaga kundendeko mwina angakaphunzireko chikhalidwe

  7. Tingokhalana nawo pansi kut asiye cikhalidwe cimeneci,bola ngat sakutenga ndi mbewu yomwe or report them to the nearest police station,or the gvt shud set an inquiry comision

  8. MZONGOFUNIKA KUKAMBIRANA SIDZOCHITA KUTENGERA AGALU KAPENA MKONDO MZAPACHIBALE.UNDUNA WA DZAULIMI UYENERA KUFUFUDZA NGATI MINDAYO YOMWE ANTHUWA AKULIMA ADAITENGA MOSAWABERA ABALEWA

  9. Mukufuna azidya chani anyaniwo? Chinangwa chomwecho mpaka kuchita kuwakumba, kuwalengeza pa social media ngati aba ndalama za cashgate?

  10. Scaring them away with dogs or just guarding the farm is a solution. Mvula ikagwa kwambili tidandaule njala, ikachepa tidandaule njala, ndi anyani omwe adzikhala pa list yoyambisa njala abale??

Comments are closed.