21-year-old man rapes 3-year-old

Advertisement
Rape Malawi

Police in Lilongwe are keeping in custody a 21-year-old man for raping a three-year-old girl.

According to Kanengo police public relations officer Salome Chibwana, the suspect James Boni sexually abused the girl at a graveyard.

“The incident happened at Mgona and was reported by the mother to the child who said she was busy cooking when she was informed by a friend that her daughter was found at the graveyard,” Chibwana.

The child later disclosed that she was feeling pain in her private parts and when the mother checked her she saw blood on the child’s private parts.

A test at the hospital confirmed that the child was raped.

The suspect was later arrested after being identified by the victim who revealed that the 21 year old man took her to the graveyard where he raped her.

Boni who is expected to appear before court soon comes from Thekerani in Thyolo district.

 

Advertisement

85 Comments

  1. Ngati nizizimba mmmmm anakunamizani.kodi ulibe wako mwana kuti umupange zimenezo?ngati ulibe upeze wako masiku otsiliza kuvomereza nibwino tili pa deport.

  2. Choncho nkumati a police ndioipa akamakuthilani unyolo, zinthu mukuchita kuziamba nokha, ngati khalidwe lako lili lonunkhalo osakangokoka Hule bwanji? chimakgala chili chani? Umfiti? kukhwima? kaduka ugong’oli? Asakusiye ndithu iwe akukakamile basi.

  3. Its very pathetic,sad ,shameful and total madness.Government should find other punishable means apart from jail sentences,such people like staying in jails coz they enjoy there Edina WaRodney Shaba Mphangela Moyo Angela Fredrick Lukhere Fortunate Watsopano Lambulira Kondwani Mc-Iver Tole Rodney Adrian Shaba Love Wa Benjamin Shaba Benjamin Shaba Grace Jackson

  4. akukulu nyeleyake yotani mpaka 3ye mahule osewa àaaaa kkkkkkiiiii ochipa mahule 250zikumatheka vutukamfusa ndiciani zopusa simwanawake

  5. Ngati kuli kufunafuna Ka virgin koti mukayambe nokha aponso mwaonjeza,kungovomereza kuti mavirgin anatha basi

  6. Ndizomvetsa chisoni, nkupanda nzeru kotani mpakana mwana wa zaka zitatu? I think he z crazy, and he must suposed 2 receive a red card!

  7. Happiness is all am experiencing now as am posting this about Dr Abuu the man that God has been using to heal people, and I and my Husband are one of them because we are cured from hiv/aids by his medicine, if not for God and Dr Abuu my children would have been orphans today but i thank God and Dr Abuu for saving my life, for those who are passing through the same should call or whatsapp Dr Abuu on whatsapp with his number +2348066454364 OR EMAIL [email protected]

  8. The problem is that you aint giving them stiff punishment…..give life imprisonment….30 going up…….osati tima seven years …10years….amunawa satana waakhalira kuzinthu zawozo

    1. Napepe achimwemwe….but its too much… dats wy mutiyankhulisa pambali?….three years zooona …mwana wanzako…..atakhala mwana wanga sangakafike wamoyo kupolisi…nzowawa kwambiri chiwewe chamtundu wanji…three years zooona…..dzana anali wa seven years…kubeleka kumawawa kuti wina azangokuonongera mwana kopanda chisoni

    2. Komaso anthufe tisama yembekezere ndende kuti ikoza zithu ma moster tikuwapanga creat tokha azimayi tikuvala mosazilemekeza pomwe tikulera mwana wa mwA muna pakhomo muganiza akapita kunja akakhala ndi khalidwe kwa anthu oti sachibale ake ?
      Kapena tinayiwala kuti anthu ena umunthu mulibe
      Charity biggins at home
      Zimawawa ana adzaka zochepa kupangidwa chipongwe chonchi chifukwa choti munthu wa mkulu wwa mzeru zake kukanikani kuganiza kuti ndi mwana mpaka kuika chikatundu chake

    3. Are you telling me mwana wa zaka zitatu ndi mzimai……kupusa chani?…….waseven years mnyamata wagwiriridwa ndi mzibabo wa 37….vutoso apa ndi la azimai mwina kuvunda akatundu anuwo….stupid idiot

  9. umfiti chyani amvapo chyani bvoa wa misala nayeso poti ndi munthu koma mpaka 3yrs? dziko silingalemere azibambo mukuvulila ana

  10. I hope Malawi has the death penalty for animals like this!

Comments are closed.