Bambo wa danzi apezeka ataphedwa ndi kudulidwa mutu ku Mulanje

Advertisement
Mozambique Bald Men Attacks

Apolisi a mu dziko muno achenjeza a Bambo onse a danzi kuti aziyenda mosamala zitadziwika kuti Bambo wina wa danzi achiwembu amupha ndi kumudula mutu mu boma la Mulanje.

PoliceApolisi ati Bambo wina wa zaka 86 amene anali ndi danzi anapezeka ataphedwa ndi kudulidwa mutu ku Mulanje. Iwo ati anthu achiwembuwo anakamutaya mu chimbuzi atamupha.

Apolisi ati agwila mnyamata wina wa zaka 23 pokhudzana ndi nkhani imeneyi.

“Padakali pano, a Thyolani Khoriwa a zaka 23 atsekeledwa mokhudzana ndi nkhani imeneyi ndipo anzawo ena awiri akufunidwa ndi Apolisi,” mneneri wa Apolisi a James Kadadzera atelo.

Nkhani zopha anthu a danzi zayamba kudziwika kuyambila pamene boma la Mozambique linachenjeza kuti mu dzikomo anthu achiwembu akusaka mitu ya danzi ati ndi chikhulupiriro choti muli golide.

Sabata ziwiri zapitazo, Apolisi ku Mozambique adanena kuti anthu a ku Malawi ndi ku Tanzania ndiwo akutsogolera khalidwe lonunkhali.

Advertisement

295 Comments

  1. guys to have baldness it does not mean that some one has possessing gold iam really touched and iam not sure that its indeed happen in mulanje but its like that lets play hard for them .they are also people like us ,we have to respect their rights .my God please help us to fight for rights of our friend who are in serious temptation i know for themselve its really difficult handle this situation off but ur miraclious present willbe of great signicficant ,effeciency ,effective and answerable to them and to the entire country amen.heiveesent r uslike e that

  2. Thank U 4 Notice This Kuliona Mmene Dziko Likuendera Kungatisinthe Muzambiri Somehow Unyamata Ndi okomedwetsa Ndi Zadziko

  3. This is all coming of our Lord Jesus Christ, satan knows his time is near, he now demanding his egents to do all these kind of nastay and evil things, tidziwe ichi onse akupha anthuwa akutochita kutumidwa ndi athu achuma chawo, ndipo ziwaro zawathu komanso magazi omwe akukhetsedwa m’mudziko rathu zina zikutumizidwa m’maiko akunja, remember akwawo ndi mizu ya kachere anakomana pansi, akuruakuru akuzidziwa zonsezi, koma mudziwa akakhara pa nkhate khoswe sapheka, akuteteza ana awo ndikumatuma anthu kuti adzipha adera Mighty God sees it all, mudzayankha mlandu wanu patsiku la chiweluzo

  4. Koma Malawi yeka Ndiye kaya sopano kumangopha basi anthu osalakwa zoona eeee iziii Boma lamalawi limaziwa koma samapanga kenakalikonse ndithu Eishii kungowona anthu opha anthu adasi mmm osapita nawo Ku police kumangowapha bas zikuchitika apapa ndi zautsiru sopano

  5. uli galu mulanje does not belong to tumbukas so there z no reason talking about tumbukas while lomwes are the ones found in mulanje where they have killed a person umbuli ndi wanu amakuletsani ndani kupita ku school

  6. Pakufikanso massive awareness campaign apa before its out of hand again!
    I think Government should do something real quick and community leaders and religious leaders should be part of the campaign

  7. Munthu ndi opatulika pazolengedwa zonse anamulenga mmchifaniziro cha Yehova palitsoka lalikulu kuganiza kuti kulibe Mulungu koma chilungamo chake Mulungu alipo ndithu ndipo ndi Mulungu oopsa pa Ulemelero wake palibe ngakhare mmodzi pansi pa thambo ili angakwanitse kuima pamaso pake koma kugwa kumapazi ake Lekani kupha abaleanga ganizilani Yehova!

  8. What’s wrong with Malawi. Pathetic issues over and over again. Does the government exist to tell all sane Malawians that killing fellow people due to beliefs is evil, and never make someone rich/or better in this cyber age. Come on…Where is the Malawi government on these issues? Terrible of the the still dark ages Malawi, if such is true!!!!!!!!!

  9. is
    not about umphawi
    or that they seek for rich all what i know is ufiti basi ndiomwe wafika povuta
    but remember kuti Mlaliki akuti
    zonse nzachabe
    Coz Mulungu azayimba mlandu za izi pa tsiku lomakiza do not think that we are the clevers

  10. Nothing to say even my cheeks hot tears stop burning me,why?we listen to evil news always.Pple still believe in idols,wealth and famous.Do u think God is sleeping?Do u think God does not see all these things?Do u think u r clever?No u r making a mistake but because we are not belong to this world,I surrender my life for the sake of God.

    1. Watch your mouth broh next time will be your father or child remember danzi limabwera olo utakula kale so u better zip ur mouth than talk like this

  11. nchifukwa chiani tsamba lino limakonda kusindikiza nkhani zabodza ife tili ku mulanje komko tatiuza mbali yomwe kwa phedwa munthuyo kt tikaone amalaw nthaw zonse timafuna kunamiza azathu ena omwe ali kutali cholinga chongofuna kuipitsa mbili ya dera

    1. Iwe Balala,this Only Issue Is True,tsambali Amalemba Zowona Vuto Ndinu Anthu.Makulini vge, Mj Boarder Pali Msewu Wa Chiringa Mutenge Umenewo,mukapeza Mtsinje Wa Mloza Mukadutsa Gawani Ss,b4 Likanani Cdss,mukafutse.Thanks

  12. Hahahaha its funy… When u think of a human head consisting GOLD… But also pathetic when u think of these tragedies…. Killings and stuff…

  13. Kwa amene musakukhulupilila khulupililani nkhaniyi ndi yoona ndithu. Ndipo ophedwawo anali amalume anga a mmudzi mwa Makuluni TA Njema mboma la Mulanje. Timawati bambo Khonanga Makwete ndipo anali a dadzi koma okalamba ndithu. Malemuwa amasungidwa ndi ana awo ndipo amagona okha mu kanyumba komwe amagonako. Kucha kwa Monday mnyumba mwawo munapezeka magazi koma iwo munalibemo. Anthu anawafufuza dzuwa lonse koma sanapezeke. Thupi lawo linapezeka Tuesday mu chimbudzi chokumba cha nyuwani pakhomo pa banja lina koma lopanda mutu. A police anatenga amayi a pakhomopo pomwe anawo omwe amatchuka ndi khalidwe lakuba athawa. Mayiwo ndi omwe akuwulula zoti ana awo ndi omwe achita chipongwecho akuti anapeza nsika wa mutu wa dadzi. Tikunena pano mayiawo ali mmanja mwa police ndipo anthu okwiya awotcha nyumba ziwiri za pakhomopo. Chabw a Malawi14 angoyifotokoza mwachidule koma nkhaniyi ndiyoona

  14. Nothing to say poti nanenso vuto langa ndilomwelo…rip

  15. Dziko la pasi chop money ndichomcho komaso kumakumbuka tsiku lakutha moyo wako. umadula mzako mutu lelo usanalandile zammanja umazidikila Mulungu kumakuitana smart.

  16. Mutu atenga or angousiya? Ngati atenga mwadziwa bwanji kuti adali ndi danzi or waphedwa chifukwa chakuti adali ndi danzi? Be professional pliz. Dont only be writing things to be famous rather than popular.write something u r sure of. The truth will b known only when the murderer is cought. Osakolezera kupha adanzi pliz.

  17. If stephen aman richly blssd by GOD and full ov power performed great miracles and wonders among the ppl was stoned publicaly by members of the council ,why is it the grvment ,police seeking for aprove by bring murderers b4 court ,they shld stoned publicaly 2

    1. Komangati ndizowona Eee agalu amenewa ndiye afikapo kenakotinva kut anthu aafupi akupezeka ndi mitimaya ifupiifupi yomwe ikuyendamalonda ku ulaya komabe tingowalimbikisa anzathuopanga zipewa zamulazakuti nthawiyolemela nawoyafika apanawo agulemagalimoto chifukwakusoka chipewa chamulazanso ndintchito

  18. Kenako muyamba kupha onenepa,kenako oonda, kenako oyera, kenako akuda!
    This is bullshit, umphawi unatipweteka. We are only thinking of shortcut ways to get money. Sad

  19. A police mukumalimbana ndi ma min bus driver ndi ovala camouflage za masana izi malo mothana ndi mchitidwe umenewu ntchito yanu ndikuteteza anthu adziko lanu…umuzigwira ntchito usiku oasmangokhala pa office

  20. Dziko Lili Mmanja Mwa Agalu Tsapano, Nanga Kungomva Kuti Ndi Chifanizo Cha Mulungu Nde Akuti Tibwelere Komwe Tinachokera?? (aboma Taganizani)

    1. Boss…in most cases imakhala link ya anthu woti akukuziwa…..sikuti upandu umachitika ukangowonedwa ndi dazi NO!…ts a game plan…..anyways partially ur point can work

  21. that’s really a pathetic behaviour. but that’s not the way to prosper in life. no no no…. Malawians calm down. our colonial masters have something to do with this. I will explain. u guess their main agenda is to blindfold us. they want us to stop believing in biblical things. I do bliv that they want to lie to us. they want some pure lunatic educated people to convert us. especially these tumbuka who takes almost 45 yrs doing primary n tertiary education. we all know how stupid they are. but wait. they will use those bones n skulls to provide some cheap n shallow proofs . I don’t care what some dick heads will try to look like they r saints. the truth have been said . all my statements are normative. don’t talk trush

    1. Tribalism is not good at all,eeeee so much hatred this guy,I don’t see how tumbuka’s are related to this story,you are a human being with full of bitterness,you are a waste of resources in the universe,with the stunt you pulled here,pple will start arguing to each other

  22. Tawauzani makape apolicewo ndithana nawo akapanda kupeza wapanga zimenezi .. Koma kuba basi.. Infa yamunthu iwowo amafuna ndlama zilowe nthumba bas

    Nanuso mazoba mwaposta nkhaniy ndnu otani? Simunaonepo wadazi ataphedwa?

  23. Eeeeeesh umphawi Ku Malawi unanyanya,zochotsana maliseche ,kupha albino zatha tsopano ?zayamba zamadazi ..bwanji Ku Botswana ,Zambia ,Namibia Kenya ndimaiko ambiri mu Africa sizinachitikepo izi…

  24. amudula mutu!? nde aziwa bwanji kut anali wa dazi? anaupeza mutuwo?… guys uchifwamba uli paliponse nde akaphaso muthu wanfupi munenaso kut amupha chifukwa chakufupika?

  25. Permanent Hair Disaster(PhD) likhalenso vuto lot tizvutika nalo..? plz plz muzimvako chisoni…mwapha albino…sakukukwanani pano mwatembenukila kwa anthu adazi?? mmm almighty God will intervene & bring judgment to all people who indulge themselves in that stupid business.

  26. The next will be short pple the only way to eliminate this notorious conduct in Malawi is mob justice once caught the should face stones in full view

  27. Zachoka my Albion zafika kwa anthu adadzi?why Malawi ? Why mutharika ? Tikamange nyumba dzathu kuti komwe kili chitetedzo? Ku Area 30 akuba aba macurtain church

    1. Koma pafundo I-square tichedwepo munthu timamuzindikila kamba ka khope ndi chifukwa akuba ambiri amava mask kumaso kuti asazindikilidwe, ndiye mutu wadulidwa aziwa bwaa mmmmmmmmmmmm

    2. AMalawi muli pano kumamvetsetsa wanena m’bale wawo kut analid ndidanzi malemuwo, ndipo anali abale aked, ndeno kubweleza bweleza Why?

Comments are closed.