Breaking: Carlsberg Malawi up in flames

Advertisement
Calrsberg Malawi

Fierce fire has gutted part of Carlsberg Malawi factory in the commercial city of Blantyre this afternoon, Malawi24 can report.

Carlsberg Malawi
The Carlsberg factory on fire

According to reports, two people have been injured following the incident at the Carlsberg brewery section.

The fire which is still raging has also destroyed property worth millions.

Authorities are yet to disclose the cause of the fire, but unconfirmed reports reveal the fire started when some technicians were working at the section near highly flammable chemicals.

The incident follows another inferno that razed down another part of the brewery section some months ago.

Carlsberg Malawi has been having maintenance works at the brewery section for a while now.

This is a developing story and Malawi24 will keep you updated.

Advertisement

175 Comments

  1. Ndichifukwa Pamafunika Insurance Kuti Zikabvuta Chonchi Itithandize Zachisoni Mzoti Ngozi Zina Timachita Chokonza Anthu Ogwila Nchito Pofuna Kubisa Zinthu Zina Komanso Kuti Ena Aoneke Olephela Achotsedwe Nchito Mulungu Alowelelepo Kuti Choonadi Chioneke

  2. Its part of life, hospitals, markets, schools houses nd any other places can burn down at one point or the other. Its just a shame that some people might lose there jobs,

      1. Amen, alcohol is wicked, let it all burn to the ground! @ Pius there are 2 types of wine in the Bible, wine is grape juice and is OK, but if you leave it long enough it turns alcoholic and then you mustn’t even look at it – see Proverbs 23 KJV towards the end to explain it. Jesus did NOT turn the water into alcoholic wine.

    1. you Moussa pussy. there people working there. that Carlsberg company contributes handsomely to Malawi economy so what shit are you saying now?

  3. Thus too bad,,, something is hovering around in malawi. Day after day listening to unsung songs…… alowelerepo ambuyee

  4. This Malawi should pray hard, I don’t know what is coming ahead. No new day in Malawi, every day is the same, accident day.

  5. This Malawi should pray hard, I don’t know what is coming ahead. No new day in Malawi, every day is the same, accident day.

  6. Ndalama ndi zinazonse zopanda tchito koma mukanati athuafa ndiangati nanga avulala ndiangati mowo amawina kwambili angulazina. koma moyo sangula

  7. Popeza boma lathu ndilolephera kugula ma galimoto a ozimisa moto acompaniyi amayenera kukhala ndi galimoto yozimisa moto cause is a big companyshame

  8. I Thank God For That Ndipo anakangowotcheratu yoseyo coz miyambo 20 v 1 amati vinyo acita ciphwete cakumwa caukali cisokosa. wosocera nazo alibe nzeru. God Forbid.

  9. Chatsala ndichan kut tiziwe zot time it’s over,Malawi ulindimwai kut zizindikila ukuziona ndimaso osat kuchita kumva,zowawisa mmasiku otsiliza

  10. Tiyeni tiyankhule bwino kuli amalawi amene akugwira ntchito because of carlsberg, its a bad development to the nation.Akulipira misonkho yaikulu kudziko tiyeni tikhale ndi umunthu.

  11. ndizokumwa utalhuta nsima inu musadandaule koma akanati nkhokwe za chimanga ndie kunakakhala kulira mwana ndi mkulu yemwe masayang’ana nkhope

    1. Mowa ndi munzu wa machimo. idzi ngakhale dzhtapya dzilibe ntchito stupid. bola kumadandaula anzathu aluza miyoyo ku bingu stedium aja.

    2. opepeza sky kumaona ngati heven.iwetu umadya maeravi.astraut,cosmonot.i love a twin earth. we quark an atom.we are makin an engine to work on anti-proton.

    3. what’s wrong with you people????? aliyense ali ndi ufulu wonena maganizo ake. ineso ndigomva chisoni kuti mwinadi ena avulala koma ngati zayaka opanda ovulala ineso ndikuti # praise de Lord!!!! zimowa zanuzo zikubwelesa mavuto ambiri ndipo ndikanakhala ngati ndine Mtsogoleli wa dziko choyamba ndikanaseka kampani imeneyi.

    4. Milliam amenewo ndiye mau. ngati dziko lapasi lavulidwa msalu muzu wa machimo ndiye ndi mowa. ngati satana wamanga maziko padziko lapasi ndi pachipanda basi. maukwati akutha, nyasi zose padziko la pasi pano kholo ndi mowa. anthu ambili tikalephela mayetso tsiku la chimalizilo ndikumapita ku ng’anjo ya moto mowa.

    5. Enawa akungotsutsa fukwa amamwa Koma akudxiwa kt ukunena zowona bro mumzu watchimo ndijang’ala kuchimake kwachiwerewere ndiakachamba ndizina zonyasa zimachitka Malo omwera mowa

    6. Kuteteza ntchimo. koma mulungu akakanthadi. koma tidziwe kuti Mulengi alibe za nthabwala tsiku la chimalizo tikalila ndi kukukuta mano.

    7. KUKUONETSELANI MOTO PADZIKO LAPASI POMPANO KUTI MUDZIWE KUTI DZINTHUDZO DZACHABE NDIYE WANTHU SIMOSANKHANA KULILA MPAKA MAMINA KACHASO WAPYA. KUMVETSA CHISONI KWAMBILI.

Comments are closed.