Chakwera ndi samva mnkunkhu – Chatinkha

Advertisement
Lazarous Chakwera

Mmodzi mwa anthu odziwika bwino otsatira chipani chotsutsa cha Malawi Congress (MCP) Mai Chatinkha Chidzanja Nkhoma adzudzula mtsogoleri wa chipanichi kuti mdiosamva za amzake.

Mai Chidzanja Nkhoma ati kusamva kwa mtsogoleri wawoyo a Lazarus Chakwera ndikomweso kwayambitsa mikangano yokhudza kuitanitsidwa kwa msonkhano waukulu wa komveshoni wa chipanichi.

Chatinkha Chidzanja Nkhoma
Chatinkha Chidzanja Nkhoma athila nkhondo a Chakwera.

Mai Chatinkha amalankhula izi munkucheza kwawo pa lamya ya mmanja ndi mmodzi mwa aphungu anyumba yamalamulo wa chipanichi a Lingson Belekanyama.

Mmacheza awo omwe afalitsidwa kwambiri pa watsiapu, maiwa anati kukangana mumchipanichi inayamba kamba koti a Chakwera akutemetsa nkhwangwa pamwala kuti sangabwezeretse mmaudindo anthu omwe anawachotsa.

“Vuto ndilakuti Chakwera samamva zamzake ndiposo samafuna kulemekeza maganizo amzake, ndipo zonse zikuchitika panozi sizinakachitika achikhala kuti amamva zaamzake.

Ngati mukukumbuka bwino, nditauzidwa kuti ndinene zomwe ndikufuna ndinati ndikufuna anthu one omwe anachotsedwa kuti abwezeretsedwe mmaudindo awo omwe anasankhidwa pa komveshoni yapitayi.” Anatero Mai Chidzanja Nkhoma.

Iwo anauza a Belekanyama kuti chipani chawo chitha kuchita bwino ngati mtsogoleri wawoyu a Chakweraatayamba kumva maganizo a anthu ena. Ndipo anati mmalo mwake mtsogoleri wawoyu akupanga kuthekera kuti chipanichi chizamukondebe ngati msonkhano wa komveshoni.

A Belekanyama omwe amaoneka kuti nawoso akufuna kuti komveshoni yomwe ikukambidwayi itachitika anauza a Chatinkha kuti anthu otsatira chipanichi akuenera asakhale ndiphuma pankhani yomwe ilimkamwamkamwa yokhudza.

Nkhani yonse yokhudza mikangano ya komveshoni inayamba ndi mulembe wa chipanichi a Gustave Kaliwo omwe paokha ndi otsatira ena achipanichi analengeza kuti chipanichi chikhala ndi komveshoni mwezi wa July a Chakwera asakudziwa kanthu kalikonse.

Tikukamba pano, a Chakwera anakatenga chiletso Ku bwalo lozenga milandu kuti mumchipanichi musakhale msonkhano wa komveshoni omwe unaitanitsidwa ndi a Kaliwo.

Advertisement

157 Comments

  1. if people are used to the same method of doing things, they will try to broke any new method which comes. You don’t use one strategy of killing rats if you want to win. In football, a good coach will not always use the same prayers, that is why substitution is allowed. When you are substituted you don’t cease to be a member of the team. Give a chance to others, a win is for the team not individuals.

  2. Ngati maganizo ndioti chipani cha a Gogo tipala. Agogo anachoka. MCP ndi chipani chokhacho chime ndi cha AMalawi.Zinazi ndi za achimwene, a bamboo kapena cha Amati. Choncho Mayi mukanadekha.

  3. komadi tiwoneko chakwela mwina tiwoneko zina ndakhala ndiku votela chipani changa cha DPP koma akungaba 2019 ndidzawone chakwelayu mwina tiwoneko Ku sintha

  4. Amene amuyandikila ndiomwe anganene zenizeni za dr cakwele osati inu akharupa asakhwi mungolankhula pamene simunakhele nao pamozi mumangowaona mmanyuzi kapea mmawailesi simungaone colakwika

  5. Zomwe akupanga cha Chakwerazi anaziyambita ku galileya (ku assembless of god) busa wa chinyengo kusamva kumeneku ndiye azamva zonena za amalawi akazawina? Mundiyankhe inu masapota a puludzu inu

  6. Enafe timadziwa kale kuti mmene convention imene amayitanisa mzake uja in wat was their plan B, then she would start talking nonsense against Chakwera again! Musiyeni ndi magazine ake a blue! Zonse ndi nthawi!

  7. Chakwera ndi ndani? Kkkk koma abale mpaka ndi Nyoni wasewero lapamajiga hhhhmmmm please Achakwera sit down with your Jnrs for the good of MCP

  8. Ndimaona ngati Mai chatinkha mukanakhala Kaye pheee mukulakwisatu inu ndipo musachite zinthu ngati kuti inuyo mungatsogolele chipanichi Akutumaniwo akulakwitsani mwamva

  9. mai ameneyu phokosoli akufuna banja.muwuzeni andipeze ndimukwatila kwa mwezi umodzi wa july mphepo yakula iyi ine batchala wamkulu

  10. Mai Chatikha ndi modzi mwa anthu oziwika mu chipani chimenechi. Ngati akudabwa ndi zochita yudasi Chakwera sakunama. Ndiye ena inu mukamati Chakwera boma muli mbuuuuuu pamene amene amadyererawo akudabwa ndi zochita za Chakwera. Musathamange kumanyoza munthu ngati inu amakuziwani a chipaniwo.MCP kuwina lero amutenga Chatikha ndikumupasa mpando wabwino inu mukudya gaga ndi banja lanu mphuno ili biiiiiiiiii

    1. Ukuona ngati M C P ndi chipani chapantundu ngati DPP kapena UDF, chipani chogawanisa mitundu. Olo atakhala kuti sakutiziwa koma tikufuna chipani chomwe chizakwanilise zosowa za anthu m’Malawi monse. Ndiye kuti enanu mumasapota chipani chifukwa achambuyanu ali m’bomamo eti? Ndaonera inu #Daisoni_j_MBEWE

    2. akulu amenewa zoyankhula zawo ndichocho ndithu,zoyankhula zawo zimakhala zopanda nzeru always,amakhala ngati simmalawi kuti mwina zinazi sakuziona ayii…i dont even u derstand kuti makadetiwa amatha kumufaniza kapena kuzigwirizanitsa bwanji pomunena chakwera kuti ndi yudasi kaya bwanji?? kkkk,zimenezo zimatha kuonetsa kuti anthu ena mmutu mwawo mmakhala ngati mmayendanso mikodzo..be reasonable enough pipo..

  11. ukamalinbana ndi amisala palibe kusiyani nonse ndi amisala …… INE NDILIBE CHIPANI NDIPO POMWE NDILI INE KULINBANA NDICHIPANI NDITAYA NTHAWI YANGA ….. MUZIPANGA ZANUZIMENEZO …. ZAZIIIII NO SOAT …. SIMUZIWA AGALU ANDALEWA AMAKUYESANI NYANBO

  12. Mungatani mungatani ine nga nga nga nga pa Chakwera amene simukufuna chakwera ingotulukani mukayambitse chanu chipani, nkholokolo akutumani akuppwrteketsani,

    1. Iwe Golilah wako onyasa nkhope komaso wakukamwa kwakukuluyu ukuti peter muthalika ungayelekezele munthu mbambande Chakwela wakuti avala ngati wasokera pompo akamalankhula english kukoma kwambiri ngati Barack obama komaso ngati Dr hastings Kamuzu Banda. Umaona bwanji iweyo wekha mbambande chakwela moti ngakhale kumati president zikhoza kutichitila ubwino osati mbava ngati izi zopanda mano zapakamwa pobwafuka ngati chimpanzi

    2. komatu a chriss muka.anena azanu inunso muziziona kaye,kkkkkkk,chifukwa ngati mukuti CHAKWERA ndiwosasamba ndye bwampini kapena kuti ibu akhala otani?kkkkkkkk,zinazi koma,CHAKWERAYO unamuonapo kapena ukungoganiza or kulota..makadetii ayamba ndithu misala,kkkkkkk

    3. Kkkkk! Kodi asasamba mulipo amniri eti? Kkkkk! a Kariba mwangokula koma mmutu mulibe mzeru,muli mamina okhaokha. Kodi ukuona ngati #!nyau chakwera idzalamulira dzikoli? Ungoti phe uone,zomwe anapangidwa mu 2014 azionanso mu 2019,dikira uone,mupangidwa zina ndi zina phwanga,kkkkkk! Usovaaaaaaaaa!!!!!!!

    4. A Khoo nanunso khalani chete,palibe chanzeru chomwe mungakambe apa,asiileni amzanu,kkkkkk! Nyau sizingalamulire dzikoli,ife u dictator toto takana,tidatopa ndikudula ma card ife,31yrs koma chochitika osaoneka,mudali ndani inu popanda Professor Bingu wa Muyharika(May his soul rest in peace)? Osamangoyamika bwanji!!

    5. Kodi Bingunso anali Proffessor? Oooh you mean clowned proffessor!! Bingu anapanga chani choposela kuba ,kusowa kwa mankhwala nzipala, kusowa kwa ndalama zakunja, Mafuta oyendesela galimoto kunalibe, Zero deficeit budget,. Musamakambe za Bingu known as The master of Tribalism and Nepotism.Musiyeni anafa munthawi amene uja. kkkkkkk

    6. Kkkllkkk!! Usova ada,no chances for nyau ppo, l said,The Mighty DPP will rule up to 2080, musova a zipani za mu handbag inu,kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkl!

    7. inunso a chriss mukhala ngati ndinu mulungu bwanji inuyo,vuto la a moyanu ndirimenero,iwe ndye ukuona ngati ukuyankhulapo zanzeru pamenepa???,kaya ndiukadeti ndye uli pa chibalotu..kuchita kuonekeratu kuti ndwe ombwambwanatu..

    8. Kkkkkk! Pamenepa ndekut wachenjera? Iwe nde mbuzi mbuzi,kkkkkkk! Kape,DPP ndi boma,ufune usafune,kkkkk!! Ukangokolopa lake Malawi ase,usovaaaaaaa!!

    9. ndye ngati ine ndiri mbuzi bola iweyo tadzisankhire mamina ako ukutunya apawa,ukhala ndani kuposa galu?? chikutumbwee…

    10. mwana wa masikini ndweyo umakhala busy kumazipenta kuti upeze ya credit juti uzinya manyi ukunya apawaka,ufiti kapena chani?? kupusa! kuzolowera kupemphetsa basii! moya otheratu iwe,kununkha mphere..uuukooo!!!

    11. Kape,uzichedwa ndi opposition yakoyo,yopanda tsogolo,kkkkkkkk! Uzilimbanabe ndi galu wakuda wakoyo mpaka kale kumangokhala atsogoleri otsutsa boma basi,makape anzanu akuphaka life. Moover yemwe mmati kamuzu wanuyo komanso a Tcheya adayitembelera mcp(galu wakuda) kuti sadzatenganso boma,ndkumva nawe chisoni kuti mwana ngati iwe udakalimbanabe ndi chipani chamagazi ngati chimenechi,ulibe mzelu ase. Chipani cha galu wakuda chidachita expire.

    12. iweyo ndye chitsiru chotheratu,chipani cha magazi ndichimene chinampha robert chasowa,late njauju,nanga anthu aja munapha ku mzuzu aja? u should be ashamed urself,kuphaka life mukubera anthi osauuka?? iwenso chi bingu chakocho ndichimene china weretsa mnkhalidwe onukha ngati ukunya apawa..bakhaa

    13. iwe ukamba za tcheya mesa pano mukubera limodzi ndimwana wake,iwedi ndwe opusa zinthuzi siuzitsata etiii??kkkkkk,ndimaona ngati ndwe ozindikila koma shaaaa…mbalame yotheratu,tcheya atemberera bwanjinso mcp,tcheya anatemberera chipani chake cha udf kuti chidzatha ngati makatani,pani ndichimene mukubera nacho limodzi..kuthadi ngati makatani..koma shaaa..

    14. aa ndakuona kape iwe,kodi ndiwe mbwengo waku kaya,ku chiweta,SIBWENI (in capital letters)? ndaleka kulimbana nawe,wakwithu munthu wakuda kwambiri,oyera kumtunda kokha. Mtumbukadi simunthu,kkkkkkkkkkkkkkkkk!!! tazingolima fodya kumeneko

    15. ngati uli munthu ikatu pic yako anthu aone kuda kwakoko,kkkkkkkkkkkkk! uudziwa kuti usekesa anthu,kkkkkkkkkkkk!!!!!!!!!!!!!!!!!

    16. koma shaa,u savage wake ndiumenewo,ukungolimbana ndi mitundu ya nzako ngati kuti mtundu wanuwo ndiye kuli ophuzira bwanji??,pano ndikunena pano ine kwathu watchito ophika wakwanuko,mulonda wakwanuko,kuchita kuvetsa chisoni..chabwino timalima fodya ndikulemba dzianthu dzakwanuko kumatilimira,kumatiwetera ng’ombe..kwanu nanga azitaniko…think not just mbwerera ukiyankhula apazi,ndikuti kumene kulibe anthu akuda??? palibe cha nzeru chimene ukuyankhulaponso apa ndipo ,ur jst full with hatred basii…

    17. kkkkkkkkkkkkkkkkkk!!!! koma mbwengo uyu,ndiponso iwe,ma wakwithu chipani chanu nchiti? ukulimbanatu ndi zipanu za amzako,nanga kumpotoko mmathawako chifukwa chani nkumabwera ku BT? Ukudziwa kuti si kumalo ikokhala anthu,city of a very BLACK PEOPLE like black polish,kkkkkkkkkkkkkkkkkkk! Chiputulaaaaaaaaaaa

    18. kkkkkkkkk,ukamasewera ndi nkhumba nawenso umaoneka ngati nkhumbayo,nanji nanji uzituamangitsana kapena kuzewera ndi wamisala anthu amatinso ndwe wamisala,ndasiya,ine am jst a human being ndye ndikuona kuti ndikulimbana mbwantasa otheratu…by the way blantyre muli anthu obwera ambiri iweyo uziyankhula zakwanu kweni kweni…pusiiii…

    19. Hahaha bola kuvala nyau nanga ndi Amai ako aja amaonetsa dzimabere ndikumati mlankho wàlomwe?hahaha savage tribe in Malawi .mwana wahule iwe.

    20. #AlexenderKabichiKalengamaChitsulo zovetsa chisoni ndizoti makapewa amathawa kwao kumwera chifukwa cha njala kumadzalima utenanti Ku kasungu, mchinji komanso ndwangwa (nkhotakota) ndiye dzikatero dziyambe kunyoza achewa ngati zamzeru.mtundu wachilomwe ndi omvetsa chisoni , azimai akuluakulu dzi mawere matundu ndiye mkumanyoza ngati zenizeni.kkkkkk savages.

    21. Stupid guy J Kay you are even failing to write one sentence hey. plus u r dissing most good looking tribe in Mw , are you mad? don’t show ur stupidity here or otherwise come and kiss my ass

    22. Hahaha most good looking tribe, kkkkkk mboni ndi chaponda ndi Peter muntharika kkkkkk probably ugliest tribe in Malawi.

    23. Panga zaine ,kkkkkk kape ngati iwe ungapusitse ndani #chrissRichard.kkkkkk ukoma kwake ndi makudziwa ndikuntyola nkwiko ndikakupeza.

    24. hahaha koma ndi kaprofile pic kamene ulibe! ur Fb profile is incomplete and it’s just showing how ignorant u r. nthawi yomaika macelebrity as ur profile pic inadutsa kalekale nthawi ya Bingu u better shut up ur mouth u ugliest boy. u can’t even make one simple sentence to comment instead what kind of xul did you go #JKay?

    25. Hahaha koma akapolo inu munafatsatu kkkkkk ndiye profile pic ikukhudza chiani kape iwe? Kkkkkk iweyo unapita kusukulu kunyasa kwake kumeneko? Ati inapita nthawi ya bingu kkkkkk I checked your photos ,you’re one ugliest lomwes indeed.don’t talk about xul poorest nigga ,ain’t your level .go & suck lomwes bitch pussy who expose Breast in public. Stupid low life bitches.

    26. Ada John,usalimbane ndi mwana maskiniyi #jkay akufuna pofera changa ameneyi,moover ndi munthu onyasa mwa onyasa onse(among the nyau and SIBWENI’s). Ufera za eni phwanga,pomwe pachoka nkhani sukudziwapo kape iwe,mxiew!!!!!

    27. kkkkkkkkkkkkkkkk!!! nde kubesatu ada,vuto lako ndi chani brazaman? kkkkkkkkkkkkkk! yakuphwaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa

  13. Mai chatinkha akutumidwa ndi a Dpp kuti asokoneze chipani cha MCP ndiye Chakwe ndipovuta kuti asekelere zopusa ngati izi

  14. ine siwandale ndipo ndilibe chipani chili chonse pa dziko la pansi koma langa ndi pempho kwa m’zimaiyu kuti mwai alinawo akhoza kungoyambitsa chipani chake kusiyana ndikumakhalira kunyoza chosecho amvala makaka ofanana

    1. Ai sichoncho, musaweluze motelomo, maiiyo simulendo, osokoneza ndi uyu muti m’busayu maiyu ndi landlodie, mkului uyu m’busai ndi tenanti aaaaa mukuganiza bwaaaa.

    2. Cytonie ulibe nzelu ndakuona choncho kodi mayi Chatinkha mchifukwa chani nthawi zonse amakhala busy ndi Chakwela? Bwanji ngati akufuna utsogoleri osangoyambitsa chipani chake

    3. ndanena kale ine siwandale koma amaiwa nthawi zonse ndikamawelenga zoyankhula zawo zimakhala zonyoza chakwela ndiye pa chichewa pali mau oti chikuni ukachiwona kuti ndi chomwe chikupanga utsi kwambiri umangochisolora tsono poti uyu mzimayiyu ndi munthu ayi kaya sanachedwe angochokamo ndiyeyu basi mkukayamba kuphika zake ndizosabvutatu izi palibeso angadabwe ayi sinanga wathawa kumsamva kwa chakwela eyetu

    4. cryton,MCP sichipani cha banja ngati mmene ili dipipi ndi udf nop,ndye chatinkha sangakhale landlord ngati chipanicho ndichake ayii,after all ndizimayi wolephera kale,kungoti chomwe chavita ndichakuti MCP panopa iri very strong moti ambiri sakugona nayo akungotsekula mmimda mwakamwazi,makadeti mitu yawo yasokonekera coz propaganda yawo ndimene ikupangitsa chakwera to be popular,hence no wonder ndi comment yanuyi…but coz its ur opinion ayi we respect it,kkkkkkk

    5. #aCassim ndinu a Mcp musaputsitse an2..izi Ndi ndale & kuli ufulu wakulakhura kunjaku..akuyenera kudzudzura ngati Pena pake sakupaona bwino mopanda kummanga Nyakula wina kapena kukamponya ku Ng’ona….

    6. Akanakhala kuti mayi uyu ndiwanzeru zakuti angayendetse chipani akanamusankha iye kuti akhale president wa MCP. Koma Mai uyu ndi madeya odyetsa nkhumba basi akhala choncho ndi mwano wakewo.

    7. #shoaib undikhulupilire ine sindimayima pa mzere kukabvotela munthu ndipo sindingachite komaso sindidzapanga zimenezo koma ndimangowafunila zabwino amaiwa kuti mtima wawo usamakhale okhumudwa nthawi zonse chifukwa cha chakwela akhoza kufa ndi bp bola atangoyamba zawo ndipotu anthu akhoza kuwabvotela chifukwa akuwonetsa kuti ndiwolimba mtima mumayankhulidwe awo nanga mpaka kumunena mtsogoleri wawo kuti ndi gung’ungu’u iwo ndiye adzakhala ndani kweni kweni

    8. chimene chimasiyanitsa dpp ndi zipani zina ndi kusakangana okhaokha openly. Ndipo ngati zipan zina ndi mzika za ku opposition ndi chifukwa choti zilibe direction ya umodzi mchipani, ndipo kukanganaku kumabweretsa zibowo nthawi yamavot. Dpp ilibe economic and social leaderships but political leadership. Udf idachuluka social leadership. Mcp idali good p economic leadership koma social and political leadership mmmm mbola. Mavuto a mcp pano akuonetsa kut president ndi omutsata ndi aphuma situational judgment ndyowavuta and ali nd false hope. a dpp ali ndi vuto lokhulupirira zawo zokha koma party and political organization excellent

    9. @shadreck banda: zaonetsa kuti sumadziwa tanthauzo la excellent kuti kodi amapelekedwa pa zinthu zotani, ngati Dpp adaba ndipo akuba ndalama zaboma komaso alikupha anthu ngati Njaunju, Mbendela, Chasowa, kutseka chanco komaso kumenya ana aprimary kamba kakuti akuumiliza boma kuti lipeleke ndalama kwa aphuzitsi kuti anawo ayambe kuphuzira ndiye choncho pali chifukwa yowayamikila kuti zilibwino ndipo excellent?

Comments are closed.