Malawian girl resurrects after 20 years

Advertisement

People in Mulanje have been engulfed with disbelief  after a girl who died 20 years ago reappeared in the district on Wednesday.

Mulanje Police Spokesperson Gresham Ngwira has confirmed the development with Malawi24.

Back to life.

According to Ngwira, the lady only identified as Mercy Chibwana who is alleged to have died in 1997 while she was in Form 2 is said to have resurrected at Namulenga in Mulanje.

“Yesterday the girl reappeared and started following another woman who asked her where she was going only to tell her that she would narrate everything to police,” Ngwira said.

“When she arrived at Namulenga police unit she failed to say anything compelling officers to refer her to the nearby health centre.”

According to Ngwira, while there she started mentioning some names of her relatives which made the people to call the mentioned relations who identified her through some marks on her body.

Currently she is at Mulanje district hospital for further treatment.

Advertisement

282 Comments

  1. Iyi si resurrection chifukwa resurrected munthu sakhala ndi mafupa fufuzani liu loti mugwilitse ntchito Resurrected Munthu amakhala Ghost iyo ndiyo Resurrection

  2. All Who Are Saying This Cannot Happen Definately You Have Never Visited And Stayed In Mulanje. That Is A Magical System Called Ndondocha,they Use These People In Farms.

  3. people confused on the word “ressurrection” may be you should not use this word, coz if you can go to her grave you will find may be no way out, why Jesus’ tomb a heavy rock opened, so this one was just somewhere magically.

  4. This is all nonsense! Why do Malawians believe in such crazy stories? Truth is that once dead and buried then a human being ca never come back to life. This is more fiction than fiction!!!!!!!!

  5. Izi zikhoza kukhala zoona ndithu kunoso ku ntheu zachitika mwezi wathawu amakhala kuti munthuyo sanamwalile ayi koma anangosowesedwa mmatsenga khulupililani ndithu zikuchitika izi

  6. Girl usaone ngat yelusalemu wasopano uja nduyuyu ai.izi ndi chito zasatana mmene zikugwilila tchito, ndiganiza utamwalila amalume ako anazalemba kalta kuziwisa zamalilo ako ku tauni selfon inali yosow, ground fon inali ku boma, meshi zophoda ndi zonyezmila ndi zo sekemela zalelo usazilondole ndiye chionongeko cha moyo uno, ungoyang’ana panta wa yesu kut ukapulumusidwe mu chilango chili nkuza.

  7. She did not die after all She went miss ,If she was dead her body was supposed to decompose. Maybe witchcraft take place mufutse bwino ameneyo

  8. Izi ziliso nkhata_bay west,mnyamata anamwalira 6 years ago,koma pano akumaonekera kwa makolo ake.
    ndkunena pano akumabwera ndkumapita and as for now akumamu siira nsima yamazulo ndikuiika pa( chitanthali in my Tonga language) poyanika mbale.
    usiku amabwera ndkuzadya nsima yemwe amamsiirayo.

    Anaulura komwe akumamusunga ndi omwe anamuzembesa magically, ndipo atafusidwa afitiwo anafomelezs,analonjezaso kut azamupeleka chifukwa akuwavutisa,komano atafa tinamu kwirira

    Anapha eti ndkumu tumiza Ku jowen kuti mwana wawo azika landira kawiri pamwezi,komano man yaku joweniyo inamkana eti coz anali friend wake

    Tikudira tsiku lomwe afitiwo analonjeza kuzamupeleka ndipo ndikaona nawu

  9. kunoso Ku ntcheu zachitika .mzimayi anamwalira mchaka cha 2001 wabwera Ali wamoyo .pano ndinena ali kwawo kugwira ntchito zapakhomo.akuti anamwalira pa ntcheu district hospital as she was derivering her baby.

  10. #Inno you are aliar , which bible do you use ? Jesus raised the dead and not him never heard of Prophet’s bones which raised a dead person ?

  11. The same case happened in Tcheu, Mlanda where a woman died in 1986 came back to life in 2006 & she explained clearly that she was alive by the time her

  12. Kutereko simunamveko zangati zimenezi zitachitika???
    Zakhala zuchitika mobwereza bwereza izi

    Usually it’s connected with black magic,the person could have been put to death by the powers of charms or rituals I may say it that way then after the rituals expire its when the dead can resurrect SIMPLE AND STRAOGHT FORWARD
    Why urging like you ain’t sons and daughters of mother Malawi where magic still in practice

  13. with wichcraft this is possible.the real body is that resurrected one,that which was burried was just a her shadow.we have experienced similar cases like this. to hell satan

  14. with wichcraft this is possible.the real body is that resurrected one,that which was burried was just a her shadow.we have experienced similar cases like this. to hell satan

  15. what evidence do they have that its realy the girl that died.did they go to the graveyard and check whether bones are missing or not? or did they do DNA testing to realy make sure they are related with the family.A malawi tisamango khulupilila zinthu ngati ndi make dzana kulibe science. wake up

  16. That will nevver happen .She is just resembling the one who died.Nobody will resurrect apart from Jesus who resurrected bibilically.But scientically no one can. She should be examined mentally.

  17. is she not supposed to look old counting the 20 years that has passed

  18. Welcome back!! wapeza dziko litssintha, kuli fb, watsap etc. zakumwa zozizira zatsopano eg fronzy. Team ya Bullets umasapota ija pano ikungoluza, uiwonera wekha sunday likubwerali ku mulanje konko. tinalamulidwako ndi mzimayi mdziko muno. a president anafako ali paudindo. zina ukuuza ena

    1. Kkkkkkk anthu inu mzathu yi mwamulandiladi ndaona chomcho. Ayi ndikofunikadi kumuuza zina ndi zina zomwe zachika iye kulibe.

  19. u pipo,we had a similar story here in zambia,but it ended without proof.they went to exhume the grave and found a skeleton of their dead.it ended up as mistaken identity

  20. guyz nd zoonad koma?muxakhale mwakoka nazi nde nkumanamza anthu y.ngat nzoona pelekan nambala ya doctor,polce or amfumu a mmudz wawo

  21. Ngati ndizona ine ndinafunitsitsa atazafotokoza ekha pa programme ya zilipati,chifukwa anthu enanu aaaaaa idont trust them.BOLA NGATI AKUYANKHULA.

  22. Sanafe ameneyo,bcuz whn o livin tinz e.g anthu,dies,decomposes&bcomez manure,how possible iz it tht she must come out bwinobwino,is her graveyard still intact?..anatulukila pati,kapena ngati anatuluka yekha how dd she manage to kick de soil&coffin out?..zaboza izi,i will only bliv if sum1 dies,ressurect&bcome azombie.

  23. Kumapemphela- anzathu omwe adamwalira madzana azaka zapitazo, mpaka lero adakali m’manda. Thupi lawo lidakhudzidwa ndichilakho cha matenda, moyo unagonja ,

  24. tsikanayo Anamusowetsa Mumasenga Ngati Kuti Wamwalira Koma Anali Atamutenga Ndikumakamugwilitsa Ntchito Zolemetsa Mumasenga Mwaomo. Bambo Yemwe Anapanga Zamasengazo Anamwali Ndipo Zinthu Zonse Anasiyira Mkazi Wawo, Ndiye Tsikanayo Wapeza Mwayi Wothawako Pamene Anzake 5 Adakali Konko… Kwavuta Kunamulenga Eti Afukule Manda Ake Kuti Apeze Umboni Weniweni

  25. Pls tell us what really happened?atiwuze kuti anali kuti?cz guys ufiti mst be a true thing,but im glad shz bk wt her family at last image th trauma sh mst hav gone thru

    1. Ndizoona aseh. I have relative komkuno ndi nurse pa mulanje hospital.. Wacheza naye.. Of course tym imeneyo ati samalankhula bohbo. Coz amakhala ngt wasokonekera.. Kma abale ake anali konko

  26. Malawi51, have you followed the story to the core? Could it be resurrection? Really?

    I’m quite sceptical. Only Christ Jesus resurrected, the rest of us are doomed, thanks to Eve’s sinning against God. Death was given to us as a punishment, we must die and never wake up again someday.

  27. Eeeeee aise ndye wafkira mmavuto2 ingobwelelan man dziko linaipa ili, : amuna akukwatana okhaokha, anthu kuphana, achuma akungozilemeretsa, milandu ikukomela achuma, just few! Anyway uziona wakula watha

  28. “Glad to know that She has been alive all the past 20 years”.She will die for real one day,just like all of us will.

  29. Koma Brashyo yobaya iyo ili mmutu mwakeyo ndi momwe adametela mu 1997 yo kapena mwamumeta waukamo? Nkhaniyi ndiikhulupilira ngakhale zaka zikuchuluka koma poti mwaika maina a mapolisi officers, ma health center komaso polisi unit , ok amulandile koma abale ake akawadziwa eti?

    1. kkkkkkk apa ndiye wayithatu mwina tipume poti ndabva kuti wawabweletsela magolo aja anasowa ku bullets aja lipipa umayitha kkkkk

  30. Yes ndizoona ndipo dzina lake ndi Mercy Chibwana,anabadwa muchaka cha 1979 ndpo anamwalira muchaka cha 1997….Padakali pano akumupima pa chipatala cha boma ku Mulanje

    1. Kmano anazindikira bwanji mudzi wakwawo iyeyo n atamufunsa walongosola kut zakhar bwanji kuti apezekenso akuyenda pa dziko pano

    2. Yes anaikidwadi mmanda koma chodabwitsa ndichakuti wapezeka ku Nkando ndpo anapita ku police ya Namulenga..atafunsidwa walongosola kuti zaka zonsezi anali mushop ina mu Limbe mumzinda wa Blantyre…Komanso anakwanitsa kutchula maina aabale komanso achibale atayitanidwa abvomera kuti ndi m’bale waodi

    3. Wina akuti sakulankhula. Wina akuti akulankhula. Timve ziti ziti? So far amene anauka kwa akufa anatero mu nthawi ya Yesu basi (Yesu mwini, Lazaro ndi kamwana kakakazi kaja).

    4. Musanamizidwe kuti sakulankhula…anakakakhala kuti sakulankhula apolice akanadziwa bwanji abale ake,kwao komanso komwe anali nthawi yonseyi….Kumeneko ndikwathu thats y ndakwanitsa mpaka kutchula dzina lake komanso mudzi wake

    5. #ANN_MSOKERA… mwati sakulankhula kalikonse..
      #PAT,,naye akufotokoza monveka bwino kt kupolisi mun2yi wazifotokoza bwino lomwe…
      #TITSATE_ZITI???
      nanga wa shop ku limbe yu,akumufotokozanso??

    6. Mwana amene anabadwa 1979, panopa ndi amayi azaka 38, ndie muthui wabwera ali mwanabe analiko samakura, izi ndi zaboza muthu akakwililidwa samazukaso ayi, ameneyo amachedwa kut, (zombie)

    1. if u r in Mulanje does nt mean u can know everything happening in the whole district, mwaona ena akuwuzan za mudzi kwachtikira zinthuzi inu simukudziwanso pamenepa wakhuta tsabola waa mwenye ndani?

    2. Iwe usawachititse manyazi alomwe amzako!!! kumangotsutsa zopandapake basi..
      Argument yako yofoila heavy….
      mxiew!!!! ndaBoweka nawe

    3. iwe osangonkhala chete bwanji iwe ngati kulikwanu ifenso ndikkwathu koma tikudziwa kuti mulanje ndiwamkulu dzedi ndipo sitingadziwe madera onse ayi nanga iwe kwanu ndimulanje yense? chitsanzo ine kwathu ndi mulanje border koma sikuti midzi yonse yaku border ndimaidziwa ayi nanga iwe munthu odziwa mulanje yense ndiwakuti dela lakwanu mwinanso ine mulanje ndikudziwa madela ambiri kuposa iwe from mkando ulendo mzizila uyo mpaka kwachinyama mbowela msika wanjala chisitu kwansona kwagawani and many more kuzungulila mulanje koma or half mulanje sidamdziwe ayi

    4. and munthu ameneyi kwao ndikuphiridi onyamula nanazi kutsika nawo phiri kudzagulitsa ku minimini ndiye ukadziwe zakwajuma mwina iwe umauluka usiku boma lonse kuti udziwe zamulanje yense

Comments are closed.