Three headless bodies identified

Advertisement
Chikwawa

Three bodies of people that were found in Bunda forest last month have been identified, Malawi24 can report.

The bodies are said to have been of headmaster from Monga Primary School in Rumphi district Dalious Chawinga aged 42, his wife Queen Zgambo and a 5 year-old daughter Olipa Chawinga.

According to Lilongwe Police Spokesperson Kingsley Dandaula, the family left Rumphi for Lilongwe where they had planned to buy a family car on 9th April.

A relation to the family Mabvuto Chilembo said the family told their relatives that they had succeeded in buying the car and they were registering it at Road Traffic.

Reports suggests that car sellers might have had a hand in the brutal murder of the three.

The three are to be buried at Chilundika village, Traditional Authority (TA) Chikulamayembe in Rumphi.

Advertisement

181 Comments

  1. very bad,mizimu yawo iunse my mtendere anafa imfa yowawa anthu awa kufa family yonse? kumfa ngati ziweto? Mulungu odziwa kutothonza mwini zifundo Tonthozani banja lotsalali In the name of Jesus Ame.

  2. Buying vehicle in Malawi is it something major in life or what l wonder why u killing each other coz somebody buy himself or herself vehicle…Shame poor Malawi..and its people.

  3. Pepani Malawi .mwinatu ndi chimanga chomwe tikudyachi chimene akugawa kuchokela kwa Bushilichi ndiye akufuna abwezelese pomwe akuchosa.Eashiiiii.

  4. Ndinu nomwe anthu akumalawi omwe mumati osamapha mbava.koma taonani kodi zidachitika apa ndi umunthu? zovetsa chisoni.anthu kuwadula makosi ngati nkhuku.adalakwa chani?NDE MUTAMABAKILA MBAVA. KODI UBWINO WAMBAVA NDI UT?

  5. Since the bodies have been identified now the remaining task is with the police to catch the culprits. And i am sure that our police is very competent that it will not take long to bring the culprits to book .Things like analysing the call log of the deceased may give the clue to apprehend the culprits.

  6. If there is justice in Malawi thi case its easy to solve and i pray justice to previal: The culpuit is the vehicle seller cn be traced in seconds!! REST IN PEACE THE Zgambo’s

  7. Malawi is becoming a dangerous country. This is Satanism and witchcraft. God forbid. Evil people God will punish you.

  8. Killing the whole family just bcoz ov cash, mmmmm Lord hav mercy. Let the robbers b punished by God while alive aumve moyo kuwawa

  9. Komano a #Malawi24_Za _Link_Zanuzi_ayi_zikution ongera_nthawi
    Makobili Akuvuta.
    Malawi Wanunkha Mpaka Banja Lonse Sad News Koma A Componyo Mmmmmm :> ?

  10. In a Land where Faith Leaders nolonger exist & the entire environment becomes all of wild Beasts who prey on each other. A once very PEACEFUL Nation is now the Devil’s stronghold all in the name of Democracy & Human Rights. (making evil look & sound pleasant).

  11. Ambuye yehova amaona zonse bwino lomwe ndiye sikuchenjera kumaononga miyoyo ya anthu motere mkwiyo wa yehova uwalange mwapaderadera ochita nkhaza onse amen

  12. Its very unfortunate and sad hearing about this news , The government of Malawi should look into this so that justice must prevail, Make sure these satans,monsters/beasts are brought to book

  13. R I P,
    kwa omwe sakumvetsa,,,
    nkhaniyi inalembedwapo masiku apitawo,,apa ikungopitilizidwa,,
    apolisi adapeza mitembo itatu mu nkhalango ya Bunda ku Lilongwe, koma samadziwika kuti ndi matupi andani,,,,,,
    ndiye apa zadziwika kuti anthuwo ndi aku Rumpi,,,,,,
    anaphedwa ku Lilongwe komwe amakagula galimoto,,,
    ,,,,,,,,,,,,,,,zikomo,,,,,,,

  14. Where did you do your journalism studies you Malawi 24 journalists? just close this page if u think you are not ready to write well cooked stories! Ndakwiya

  15. Muphuzire kuremba zoti anthu aziva kapena mumarota kuzorowera kurenba zandare mkhani simukuyidziwa mwaremba kale kupusa eti

    1. Anthuo anaphedwa mu mkharanga ya bunda koma mitu anaribe nde panopa adziwika kuti ndi a hedi akumpoto ndi akazao komaso mwana nde awawa anaremba ngati zachitika dzuro

  16. very sad..amfa imfa yowawa mpaka kuzinga ngati nkhuku?eshii bola akanangolanda ndalamazo kuwasiyira moyo..moyo ndi waulele kwa wina aliyense

  17. Very disturbing news!!!!
    The three beheaded bodies who were found in Bunda forest have finally been identified as a 43 year old Mr. Chawinga of chiundika village in Rumphi, a headmaster of a school, his wife and their 5 year old daughter.
    The three left Rumphi for Lilongwe to purchase a family car on 9th April. After successfully purchasing the vehicle, they informed their relations that they are processing registration at road traffic directorate. Little did they know that, that was the last communication. The bodies have been identified at Kamuzu central mogue yesterday.
    The vehicle in question is still not yet known. It seems the vehicle sellers have a hand in the ordeal.

    1. Anthu ena amarimbikira kuremba zinthu kuti anthu ave koma kukanika kufotokoza moveka bwino big inuo nde mwafotokoza moveka bwino enawa afotokoza ngati zachitika dzuro akujambura mnyumba koma zinachitikira kumkharango

    2. Nkhani ndi link apa ambiri simukuitsegula George wangotenga zomwe Malawi 24 yalemba sanasithepo kathu then your thanking him for narration ???? instead thanking him for sharing you what is in the link.

    3. Komad athuwa zikükhala ngat ãmakagula galimoto koma anapangidwa chipongwe kmabé mulungu walowéreLa kale pa nkhaniyi achitapö ka2

    1. Be active man, i can’t blame u bcz u like kumvera mbc radio. Tamaveraniko ma radio enawa simuoneka opusa ai mdzamva zambiri za dziko lanu big man.

  18. Here in Malawi usually we r killing each other for success ,pempho ndiloti wakupha nzake aziphedwa kuti mwina mchitidwe onunkhawu utheletu,munthu sungagwile ntchito molimbika kuti ulandile mphoto ya imfa,kumpha banja lonse?alandile mphoto ya uchimo awo akumphawo komanso ngati anali ogulitsa galimotoyo nde kuti sanali yenkha (just thought ) mwana waphedwayo sitikuziwa kuti mawa lake lidali lotani komanso makolo akewo amathandiza achibale powalipilira school fees ndizina zotero mmene zatelomo zasokoneza tsogolo la anthu ambiri chifukwa nawonso amene amathandizidwa ndi banjali pa mawa adamathandizanso anthu ena,ndi chain chothandizana nde mkuwapha? Pemphero ambuye Mulungu wathu wamoyo mukathe kutionetsela anthu amtunduwu poti alipo ambiri koma patokha sitingathe, kalandileni mizimu ya abale athuwa ndikwakhululukila pa zomwe adalakwa ndi kwapasa moyo osatha chifukwa mwainu muli chilichonse khalani ndikuthekela kowatonthoza anamfedwa chifukwa samayembekela kuti zitha kutelo (AMEN)

  19. Perpetrators must be dealt with communities not police.lmean burn them alive.we dont want to stay with animals in our peaceful country.

    1. Vuto la free data ndilimenelo there is link when you open it all information is right there.Mmalo mongopepha kuti ena awelengako akuuzeni mukuyakhula mukula mtimanso kuti sizikumveka anga mwawelenga nkhani yonse.?????

  20. This family went to Lilongwe to buy their car it’s were they meet robbers cut off their heads in Lilongwe it’s not means these things happen in rumphi no it happen in Lilongwe Rip my former primary school headmaster and ur family we will miss u

    1. plz malango, may u furnish us with details of wat happened to our dear colleagues. we are also mourning with u. may their souls rest in peace.

  21. Malawi why ar u fond of summarizing story?we ar left behind we dont know wat hapned.u say 3 bodies identified.from where?pliz try to giv details

    1. These ppo went to LL to buy a car and they attacked there chopped their heads off and dump their bodies in Bunda forest.Eiiiiiish so sad!!! May their souls rest eternal peace

    1. Tingopitiliza pomwe tidalekeza last month coz zinaimila poti a Police akufufuza ma identification a wanthu omwalilawa.Komabe ndimmene wafotokozela admin munthu omvetsetsa wamva angakhale kuti waiona koyamba nkhaniyi.

Comments are closed.