A PP ndiwo adachotsa a Chilima pa udindo

Advertisement
Dausi

Boma la Malawi lati likudziwa kuti anthu otsatila Mayi Joyce Banda ndiwo adalemba kalata yoti a Saulos Chilima atula pansi udindo.

Malinga ndi mneneri wa boma, a Nicolas Dausi, amene analinso mkulu wa u kazitape mu dziko lino, a boma ti akudziwa anthu amene adachita mtopola onama bodza kuti a Chilima anyanyala udindo wa wachiwili kwa mtsogoleri wa dziko lino.

A Dausi alavulira chipani cha PP moto.

“Mwanaaa, anthu ake tikuwadziwa adachita upandu umenewu,” adatero a Dausi pothilila ndemanga pa nkhaniyi.

“Ndipo anthu ake sikuti angabisale ayi,” adaonjezela chotelo. “Anthu amenewa ndi amene anathawa atangoluza zisankho zija, pano ayamba kufuna kudzetsa mpungwepungwe pakati pathu.”

Ngakhale a Dausi anakana kutchula dzina la anthuwa, anthu akuganiza kuti iwo amanena anthu a chipani chotsitsa cha Peoples’ (PP).

“Pakali pano sitikutchula mayina koma anthu amenewa ndithu anjatidwa ndi a Polisi ngakhale abisale motani,” anaopseza a Dausi.

Mtsogoleri wakale wa dziko lino a Mayi Joyce Banda anabanduka atangogonja pa zisankho za 2014 ndipo iwo akhala akudumphadumpha ku mayiko a kunja.

A Dausi potchula kuti anthu adalemba kalatawo ndi otsatira Mayi Banda zapangitsa anthu kuona ngati akunena anthu a PP.

Advertisement

183 Comments

  1. Clueless gafment led by clueless leader. shupit.

  2. mwayamba kale mwayamba kaleee! kunjenjemeraaaaaa! yoswa hoyeeee Dr chilima woyeeeee.kumamvatu, president ndi professor.vice ndi Doctor.tulursani mbundeyo tiyione.mukodza

  3. mwayamba kale mwayamba kaleee! kunjenjemeraaaaaa! yoswa hoyeeee Dr chilima woyeeeee.kumamvatu, president ndi professor.vice ndi Doctor.tulursani mbundeyo tiyione.mukodza

  4. KD MNDAN ADZABWELEPTSE CHILUNGAMO M,MALAWI MUNO? NTHAWI YA AMULUZ AMAT ADAONONGA ZINTHU NDA AKAMUZU NDPO NTHAWI YA BINGU AMAT ADAONONGA ZINTHU NDI AMULUŽ NAWONSO A PP AMAT ADAONONGA ZINTHU NDI ABINGU.KD NDAN ANGABWERE MKUNENA CHILUNGAMO NANGA NDAN ADZABWERETSE CHHLUNGAMO?

  5. KD MNDAN ADZABWELEPTSE CHILUNGAMO M,MALAWI MUNO? NTHAWI YA AMULUZ AMAT ADAONONGA ZINTHU NDA AKAMUZU NDPO NTHAWI YA BINGU AMAT ADAONONGA ZINTHU NDI AMULUŽ NAWONSO A PP AMAT ADAONONGA ZINTHU NDI ABINGU.KD NDAN ANGABWERE MKUNENA CHILUNGAMO NANGA NDAN ADZABWERETSE CHHLUNGAMO?

  6. Kod aDPP muzasia lit kulankhula za PP,,mufuna kutukwanidwa et..? Mesa mwat zotukwana ai,, CHLIMA nd PP zkugwrzana p@.? Zopusa…

  7. Abale palibe angatule pandora udindo wa u vp, musanamizidwe no matter the storm can be. Analephela bwanji joyce, chilupha zikuonekelatu kuti ndi bingu pali great disagreements? Ndiye apa pali chani?

  8. Abale palibe angatule pandora udindo wa u vp, musanamizidwe no matter the storm can be. Analephela bwanji joyce, chilupha zikuonekelatu kuti ndi bingu pali great disagreements? Ndiye apa pali chani?

  9. Analemba ndi a dpp
    plan yao ndiyoti mpando usazapite kumpoto or pakati
    muona akafuna kusankha asankha wakumwela

  10. Analemba ndi a dpp
    plan yao ndiyoti mpando usazapite kumpoto or pakati
    muona akafuna kusankha asankha wakumwela

  11. Analemba ndi Dausi asaname ameneyo m’malo motchula dzina akutchula chipani. Kulimbana ndi PP lero kuli bwanji pa campaign.

    Nenani chilungamo a Dausi. Funso: mwapeza bwanji nsanga awawa? Nanga omwe adayatsa office ya za malimidwe, nanga opha Njauju. Aaah m’dala iwe uli shit!!

    Tikifuna chilungamo M’malawi osati kulozana zala.

  12. Analemba ndi Dausi asaname ameneyo m’malo motchula dzina akutchula chipani. Kulimbana ndi PP lero kuli bwanji pa campaign.

    Nenani chilungamo a Dausi. Funso: mwapeza bwanji nsanga awawa? Nanga omwe adayatsa office ya za malimidwe, nanga opha Njauju. Aaah m’dala iwe uli shit!!

    Tikifuna chilungamo M’malawi osati kulozana zala.

  13. Inu a DPP mwagwilitsa ntchito njira yanji kuti mupeze amene adalemba kalata?komanso amene wapezekayo dzina lake ndindani? Bwanji mugwilitse ntchito njira yomweyo popeza amene adapha Njaunju,chasowa,mbendera komanso amene adaba ndalama zogura chimanga komanso cash gate mu nthawi ya ulamuliro wa DPP ?osamakondera popanga zinthu

  14. Inu a DPP mwagwilitsa ntchito njira yanji kuti mupeze amene adalemba kalata?komanso amene wapezekayo dzina lake ndindani? Bwanji mugwilitse ntchito njira yomweyo popeza amene adapha Njaunju,chasowa,mbendera komanso amene adaba ndalama zogura chimanga komanso cash gate mu nthawi ya ulamuliro wa DPP ?osamakondera popanga zinthu

  15. Kodi mwayamba zimenezi mukuona ngati ife ana eti?.zotchula chipanizo mukunama,tchulani maina aanthu omwe amagwira ntchito yopha anzao,chasowa,njauju,matafale,anthu odulidwa mitu kumitundu ndi ena ambiri mizimu yawo ikufuna chilungamo!!!!!Kodi mukuchitapo chani inu azachilungamo?

  16. Kodi mwayamba zimenezi mukuona ngati ife ana eti?.zotchula chipanizo mukunama,tchulani maina aanthu omwe amagwira ntchito yopha anzao,chasowa,njauju,matafale,anthu odulidwa mitu kumitundu ndi ena ambiri mizimu yawo ikufuna chilungamo!!!!!Kodi mukuchitapo chani inu azachilungamo?

  17. The problem is ,there is no new blood in politics that’s why otsutsa olamura amapanga zithu zoziwa okha even Ku football association of Malawi zimangofanana

  18. The problem is ,there is no new blood in politics that’s why otsutsa olamura amapanga zithu zoziwa okha even Ku football association of Malawi zimangofanana

  19. ndale za pa malawi zimenezo kudana ndi ma vice presdent mukangowina pa elections.osangopanga kut kusamakhale vice presdent bwanji?.you are now looking for your related person kut azayimile presdent.mwa jaila heavy.mwawatola amalawi.kaya zioneka.

  20. ndale za pa malawi zimenezo kudana ndi ma vice presdent mukangowina pa elections.osangopanga kut kusamakhale vice presdent bwanji?.you are now looking for your related person kut azayimile presdent.mwa jaila heavy.mwawatola amalawi.kaya zioneka.

  21. Nkhani zandale ndizovuta kuyambira kale nde apa osavutika ndikutaya nthawi kumatosanatosana…end zandale kulibeko phindu lililonse tingapezeko…tikhale bzy ndizomwe zingatukule moyo wathu watsiku nditsiku

  22. Nkhani zandale ndizovuta kuyambira kale nde apa osavutika ndikutaya nthawi kumatosanatosana…end zandale kulibeko phindu lililonse tingapezeko…tikhale bzy ndizomwe zingatukule moyo wathu watsiku nditsiku

  23. Olemba kalata wapezeka kale,
    Okupha njauju,chasowa,ma albinos,
    Chaponda simunamupezebe kodi
    Dpp govt,total disgrâce,total failure
    You have failed us malawians

  24. Olemba kalata wapezeka kale,
    Okupha njauju,chasowa,ma albinos,
    Chaponda simunamupezebe kodi
    Dpp govt,total disgrâce,total failure
    You have failed us malawians

  25. Anthu Ongokhutitsa Zimimba Zawo Awa Olimbana Mzaziiiii Mmalo Molimbana Ndicaponda Ndi Pitala Mbava Atsizinamtole Shme 2 U!!!

  26. Anthu Ongokhutitsa Zimimba Zawo Awa Olimbana Mzaziiiii Mmalo Molimbana Ndicaponda Ndi Pitala Mbava Atsizinamtole Shme 2 U!!!

  27. Nanga ndani anapha Njauju? Sanapezeke mpaka pano? Awa mwaapeza bwanji mnsanga chonchi? Tikufuna mnene maina aanthu osatiniza zoti PP. PP ndi munthu?

  28. Nanga ndani anapha Njauju? Sanapezeke mpaka pano? Awa mwaapeza bwanji mnsanga chonchi? Tikufuna mnene maina aanthu osatiniza zoti PP. PP ndi munthu?

  29. ife khani tinayidziwa kale amamene analemna tikwaziwa and mapulani awo tukwaziwa sizinati zikubwela chilima chililma chilima ndaitana kangati musaxati sindinanene

  30. ife khani tinayidziwa kale amamene analemna tikwaziwa and mapulani awo tukwaziwa sizinati zikubwela chilima chililma chilima ndaitana kangati musaxati sindinanene

  31. PP is a party (Group of people) we want a name of a person… Mwayiwala kuti paja Cassim Chilumpha munayamba chonchi?????

  32. PP is a party (Group of people) we want a name of a person… Mwayiwala kuti paja Cassim Chilumpha munayamba chonchi?????

  33. Nangati kuli minister opanda nzeru nde ndi mr dausi zomwe akunena apa ndizopanda nzeru. Mwamusemera zinyawu nonkha kuti mwina mupeze chifukwa chomuchotsela Dr saulosi chilima. Bola nthawi ya Patricia kaliate Ali minister of information amayankha zogwila ntima. Osati mr dausi mumanja mwao muli magazi amcp.

  34. Nangati kuli minister opanda nzeru nde ndi mr dausi zomwe akunena apa ndizopanda nzeru. Mwamusemera zinyawu nonkha kuti mwina mupeze chifukwa chomuchotsela Dr saulosi chilima. Bola nthawi ya Patricia kaliate Ali minister of information amayankha zogwila ntima. Osati mr dausi mumanja mwao muli magazi amcp.

  35. When dausi speaks such rubbish, you know he’s the mastermind behind such evil. Ok, how will that impact the nation anyway?

  36. When dausi speaks such rubbish, you know he’s the mastermind behind such evil. Ok, how will that impact the nation anyway?

Comments are closed.