Inu, ati musiye kutukwana pa Facebook

Advertisement
facebook

Saliokha a Peter.

Patangidutsa tsiku mtsogoleri wa dziko lino ataopseza kuti boma lake linjata anthu onse osamalika pa Facebook, naye sipikala wa nyumba ya malamulo walangiza a Malawi kuti pa Facebook sipotukwanila.

Richard Msowoya
Msowoya akudana ndi mmene a Malawi akugwilisila ntchito makina a intaneti.

Malingana ndi a Richard Msowoya amene ndi sipikala wa nyumba ya malamulo komanso wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipani chotsutsa cha Kongeresi, pa Facebook simalo onyozelapo atsogoleri.

“Ndikulangizeni achinyamata, muleke kunyoza atsogoleri anu pa Facebook,” anatelo a Msowoya polankhula kwa ana amene asonkhana mu mzinda wa Lilongwe ku mkumano wa aphungu a ana.

“Achinyamata ambiri mukutha nthawi kukhala pa Facebook ndi kumatukwana atsogoleri anu, kodi zimenezo zipindula chani?” anafunsa a Msowoya.

Iwo anamema achinyamata kuti akuyenela kutengapo gawo potukula dziko lino.

“Palibe zomati ine ndachepa, aliyense akuyenela kutengapo gawo popititsa dziko lino patsogolo,” anatelo a Msowoya.

 

Advertisement

233 Comments

  1. ukamalimbana ndi ana amatha kukuvula buluku kapenanso kukugwira za mkabudula. chachikulu apa abwana musamatikwapule ndi ulova komanso umphawi mukapanda kusiya makani ndiye eeeh maphuzo ake akhala a gold

  2. ukamalimbana ndi ana amatha kukuvula buluku kapenanso kukugwira za mkabudula. chachikulu apa abwana musamatikwapule ndi ulova komanso umphawi mukapanda kusiya makani ndiye eeeh maphuzo ake akhala a gold

  3. Aaaa musamatiopseze mukufuna tizikusekeleran ngati mwakanika mungovomeleza bwa? Ngati mukukanika kumanga ndende ndiye mukatisunga kuti bwana?

  4. Aaaa musamatiopseze mukufuna tizikusekeleran ngati mwakanika mungovomeleza bwa? Ngati mukukanika kumanga ndende ndiye mukatisunga kuti bwana?

  5. Zazii,,,inee nde singasie,,muconstitution mulibe zmenezo,,

  6. Koma muzifunse inu mukuti atsogolerinu kuti nchifukwa chani akutukwana achinyamatawa,mukapeza chifukwa solve de problem munthu satukwana pa zabwino

  7. Koma muzifunse inu mukuti atsogolerinu kuti nchifukwa chani akutukwana achinyamatawa,mukapeza chifukwa solve de problem munthu satukwana pa zabwino

  8. Flames mmawa kuponda chikopa khalan busy ku ndi maprogram opanda phinduo president in: Mukuyetsa anthu angaope nyasizo!? Mmalo moyendetsa dziko basi kungocha kusambasamba wakuparliament kukakambirana useless story,

  9. Flames mmawa kuponda chikopa khalan busy ku ndi maprogram opanda phinduo president in: Mukuyetsa anthu angaope nyasizo!? Mmalo moyendetsa dziko basi kungocha kusambasamba wakuparliament kukakambirana useless story,

  10. Guys ndikunena poyera kuti president amene akunena chocho ndi obwera awo ku Malawi kuno sikwayo that’s why akutipanga chocho poti kukuuzani kuti muzipita kwanu mumakani muzingofa bass akufuna kuziwa zambiri za komwe anachokera agaluwa inbox me

  11. Guys ndikunena poyera kuti president amene akunena chocho ndi obwera awo ku Malawi kuno sikwayo that’s why akutipanga chocho poti kukuuzani kuti muzipita kwanu mumakani muzingofa bass akufuna kuziwa zambiri za komwe anachokera agaluwa inbox me

  12. Guyz thats a Gud advice to malawians who claim to be God fearing Nation…..”tileke kutukwana every where”..koma poti wanena Langizoli ndi president…kapena kyt munthu amene Mulinaye Bad mind mdikale…chikuoneka choyipa pa zifukwa zandale……Thats very Bad..zina kumanvako Guyz…
    Langizoli ngakhale ku church amanena ndinthu…even our parents..amatilangiza..
    anywae apakamwa powola can Argue and continue kutukwana !!!!

  13. Guyz thats a Gud advice to malawians who claim to be God fearing Nation…..”tileke kutukwana every where”..koma poti wanena Langizoli ndi president…kapena kyt munthu amene Mulinaye Bad mind mdikale…chikuoneka choyipa pa zifukwa zandale……Thats very Bad..zina kumanvako Guyz…
    Langizoli ngakhale ku church amanena ndinthu…even our parents..amatilangiza..
    anywae apakamwa powola can Argue and continue kutukwana !!!!

  14. Ali kuti pamene timava agulu inu munyumba yamalamulo anthu Ali pa Fb simakape sauzidwa satukwana sanena zoboza ayi kodi thoako lako ndiye watukwana ayi wachita zopusa ndiye alikukuwuza ya very good Malawi

  15. Ali kuti pamene timava agulu inu munyumba yamalamulo anthu Ali pa Fb simakape sauzidwa satukwana sanena zoboza ayi kodi thoako lako ndiye watukwana ayi wachita zopusa ndiye alikukuwuza ya very good Malawi

  16. Ngat president yemeyo akunyoza amalawi ine ndiye ndilekelanji kutukwana amatiyamba dala atisiye ndi umphawi wathu zimatikwanila.

  17. Ngat president yemeyo akunyoza amalawi ine ndiye ndilekelanji kutukwana amatiyamba dala atisiye ndi umphawi wathu zimatikwanila.

  18. kodi iyeyo dzikumuwawa? amaona nati iyeyo akamatitukwana pa radio kumatinena kuti ntchentche amaona ngati amalawi zikuwakomera? ifetu sitilingati akumipando akewo omaombela m’manja zinthu zoipa m’malo momuza munthuyo pamene akulakwisa kuti akhomze.olo polalikila ukazaona anthu ayamba kung’ung’uza timangoleka.

  19. kodi iyeyo dzikumuwawa? amaona nati iyeyo akamatitukwana pa radio kumatinena kuti ntchentche amaona ngati amalawi zikuwakomera? ifetu sitilingati akumipando akewo omaombela m’manja zinthu zoipa m’malo momuza munthuyo pamene akulakwisa kuti akhomze.olo polalikila ukazaona anthu ayamba kung’ung’uza timangoleka.

  20. Mukalimbana ndi ndale muzafa ndi mtima .komanso olimbana ndi ndale ndi munthu okutha ma plan komanso………….loading

  21. Mukalimbana ndi ndale muzafa ndi mtima .komanso olimbana ndi ndale ndi munthu okutha ma plan komanso………….loading

  22. Kodi mwayesa kuti ku Police kukhale koopsezera anthu kuti asamalankhule za kukhosi? This is a democratic country everyone has the right kulankhula mmene afunire! The only problem is that munangotipezerera basi a Malawife, but what you have to know is that oweruza adikira oweruza nanunso nthawi yanu ikubwera muzanjatidwa there is nothing last forever muziwe zimenezo ndiponso Oli zanuzo

    1. haaa za kukhosi zizikhala zotukwana??……khan ndiyot tisiye kuyakhula zotukwana…..i think its a gud advice for Malawian sometyms who claim to be God fearing country…….koma poti wayakhula ndi president ka pena munthu oti mumadana naye ndikale..nde mwachitenga ngat ..okhomerera pakut pakamwa panu ndipowora ndikale….anywae…

  23. Kodi mwayesa kuti ku Police kukhale koopsezera anthu kuti asamalankhule za kukhosi? This is a democratic country everyone has the right kulankhula mmene afunire! The only problem is that munangotipezerera basi a Malawife, but what you have to know is that oweruza adikira oweruza nanunso nthawi yanu ikubwera muzanjatidwa there is nothing last forever muziwe zimenezo ndiponso Oli zanuzo

    1. haaa za kukhosi zizikhala zotukwana??……khan ndiyot tisiye kuyakhula zotukwana…..i think its a gud advice for Malawian sometyms who claim to be God fearing country…….koma poti wayakhula ndi president ka pena munthu oti mumadana naye ndikale..nde mwachitenga ngat ..okhomerera pakut pakamwa panu ndipowora ndikale….anywae…

  24. Musiye kaye kunyozana nokhanokha akuluakulunu (andale) ndinu mukubwelesa chisokonezo ndi kugawikana. andale nonse ndinu zitsiru unless mtasiya ndale zachikalezo

  25. Musiye kaye kunyozana nokhanokha akuluakulunu (andale) ndinu mukubwelesa chisokonezo ndi kugawikana. andale nonse ndinu zitsiru unless mtasiya ndale zachikalezo

  26. Ngati akufuna kusiya kuva kutukana angofa mene afera asogoleri ena aja Fuck agalu sitinatibe titukana kumene muonatso pankholopano ,

  27. Ngati akufuna kusiya kuva kutukana angofa mene afera asogoleri ena aja Fuck agalu sitinatibe titukana kumene muonatso pankholopano ,

  28. ma yuthi akamashambula muzaziwe kt zinthu siziri boo.kukhomelela kwambiri nkhalambazi.zikufuna zizifewa zokha pomwe ife tikungochoma kukachasu.KODI ZIKUSIYANA PAT KUNDENDE NDI KUNJA KUNO

  29. ma yuthi akamashambula muzaziwe kt zinthu siziri boo.kukhomelela kwambiri nkhalambazi.zikufuna zizifewa zokha pomwe ife tikungochoma kukachasu.KODI ZIKUSIYANA PAT KUNDENDE NDI KUNJA KUNO

  30. Kunena zoona zake za nkhanizi ndizakuti achina msowoyawo akapita madera ena kukapangitsa misonkhano kumeneko mmalo mokamba mfundo zomanga dziko amayamba kunyoza chipani cholamula zimene achimatafe timazitengera ndikuyambanso kunyoza mopitiriza chimene chili chithu cholakwika kwambiri

  31. Kunena zoona zake za nkhanizi ndizakuti achina msowoyawo akapita madera ena kukapangitsa misonkhano kumeneko mmalo mokamba mfundo zomanga dziko amayamba kunyoza chipani cholamula zimene achimatafe timazitengera ndikuyambanso kunyoza mopitiriza chimene chili chithu cholakwika kwambiri

  32. Nde iwo akufuna azititukwana pa wailes poti ndiyomwe akugwilisa ntchito potukwanisana? Akunama. Ife zinthu tikuzimvera mafb chfkwa pawailes amakondera iwowo.

  33. Nde iwo akufuna azititukwana pa wailes poti ndiyomwe akugwilisa ntchito potukwanisana? Akunama. Ife zinthu tikuzimvera mafb chfkwa pawailes amakondera iwowo.

  34. kachikena wanyera son nyammau ndawatukananso abwere azandimange agalu amenewa akongoonga chuma chaboma ndie zikutipweteka tisatukane

  35. kachikena wanyera son nyammau ndawatukananso abwere azandimange agalu amenewa akongoonga chuma chaboma ndie zikutipweteka tisatukane

  36. Ine ndimamuona ngati ndiwanzelu munthu ameneyu, zinazi kumangomvetsela koma mukayamba kutengapo mbali nanunso mungotukwanidwapo

  37. Ine ndimamuona ngati ndiwanzelu munthu ameneyu, zinazi kumangomvetsela koma mukayamba kutengapo mbali nanunso mungotukwanidwapo

  38. WHEN A BABY IS CRYING: Thats a good advice ngakhale sindikudziwa ngati pali mnyamata kapena anyama amene amatukwana azitsogoleri pamenepapa.Anyamata amangopanga react/coment pa ma posts malingana ndiuthenga wumene wabwela.Komanso ngati alipodi ena ake amene akumawatukwana, iwowo azitsogoleriwo asathamangire kuwaopseza kapena kuwanjata anyamatawo koma adzikhala ndichidwi choti amve dzifukwa zimene akutukwanidwira chifukwa some criticisims carries positive messages.Parents are there to guid children but there are other times when parents can also learn something from children.No body knows everything in this world unless if he/she was born in Heaven.So on this earth, everybody can learn a thing or two from onother person regardless of age or academic differences.So those parents should not rush into shutting up the mouths of the youth but rather, they should try to hear what message is in their noise/cries because when a baby is crying,there’s always something that it wants to be adressed by his/her mother.

  39. WHEN A BABY IS CRYING: Thats a good advice ngakhale sindikudziwa ngati pali mnyamata kapena anyama amene amatukwana azitsogoleri pamenepapa.Anyamata amangopanga react/coment pa ma posts malingana ndiuthenga wumene wabwela.Komanso ngati alipodi ena ake amene akumawatukwana, iwowo azitsogoleriwo asathamangire kuwaopseza kapena kuwanjata anyamatawo koma adzikhala ndichidwi choti amve dzifukwa zimene akutukwanidwira chifukwa some criticisims carries positive messages.Parents are there to guid children but there are other times when parents can also learn something from children.No body knows everything in this world unless if he/she was born in Heaven.So on this earth, everybody can learn a thing or two from onother person regardless of age or academic differences.So those parents should not rush into shutting up the mouths of the youth but rather, they should try to hear what message is in their noise/cries because when a baby is crying,there’s always something that it wants to be adressed by his/her mother.

  40. MWAWUZESO PANYELO PAWO AKULANKHULA ZOPUSAZO AKULEPHELA KUPANGA NJILA ZOBWELESELA CHUMA KUMALAWIKO AZILIMBANA NDI FB PALI MZELU ?ANDIPEZE KU greytown south Africa pa min cash tyres 91 Durban strt

  41. MWAWUZESO PANYELO PAWO AKULANKHULA ZOPUSAZO AKULEPHELA KUPANGA NJILA ZOBWELESELA CHUMA KUMALAWIKO AZILIMBANA NDI FB PALI MZELU ?ANDIPEZE KU greytown south Africa pa min cash tyres 91 Durban strt

  42. Sizikugwilizana musakhangati alipo munthu amene anasegula face book Malawi muno…..nd pamakhala anthu amayiko osiysnasiyana and apa its jct a social net yochezela nd hu r u to stop it …..ngati zikumaku bhowani musamawelenge……..And go to hell……hu the hell r u….

  43. Sizikugwilizana musakhangati alipo munthu amene anasegula face book Malawi muno…..nd pamakhala anthu amayiko osiysnasiyana and apa its jct a social net yochezela nd hu r u to stop it …..ngati zikumaku bhowani musamawelenge……..And go to hell……hu the hell r u….

  44. Watukwanidwa akakambe ku Police wayandikana nayo, Pomwe amaloleza Facebook ku Malawi sanaziwe kuti kuli Anthu wosiyana zochita

  45. Watukwanidwa akakambe ku Police wayandikana nayo, Pomwe amaloleza Facebook ku Malawi sanaziwe kuti kuli Anthu wosiyana zochita

Comments are closed.