Chaponda office fire: Kalua quells fears of evidence being destroyed

Advertisement
Ministry of Agriculture Office fire

Outspoken Rumphi East legislator Kamlepo Kalua has claimed that the Joint Parliamentary Committee on the maizegate scandal has evidence on the saga which investigators can use.

This follows fears that the inferno at the ministry of agriculture, irrigation and water development offices last week may have destroyed evidence.

Some quarters have suspected that the fire that gutted Minister of Agriculture George Chaponda’s office may have destroyed evidence for the investigations that the Anti-Corruption Bureau (ACB) may conduct as recommended by the commission of inquiry.

kamlepo-kalua
Kalua: There is a serious suspicion.

However, Kalua has assured Malawians that crucial evidence on the maize deal is not only with the ministry of agriculture hence Malawians should not worry that the fire is to derail investigations.

“Aaah ayi, zimenezo ndinena kuti ayi chifukwa zonse zofunika tilinazo a Malawi asadele nkhawa zonse zilipo (aaah …no…On that I can say no because we have files containing evidence on the matter,” said Kalua.

He further assured Malawians that the country is not going to pay any money to Kaloswe Courier Limited which is suing Admarc for breach of contract.

“Kaloswe ndi company yomwe a Malawi ambiri alimo nde apanga sue kuti Malawi ilipile ma billions, mmmhuh… koma umboni tilinawo akayamba zaozo ma pepala alipo (Kaloswe is a company that is partly owned by Malawians and they have sued that Malawi should pay billions. But we have evidence,” he added.

Following the blaze, some quarters had their own theories regarding the fire at the ministry of agriculture offices but government said the inferno started due to an electrical fault.

Advertisement

32 Comments

  1. Chaponda and peter mutharika are all rotten people.If the party is rotten on it’s head and what more with it’s foot?.This ,reveals that mutharika will do nothing on maizegate scandal.Malawians let’s think of dumping the party with the president in lake malawi and map MCP with Lazarus chakwera the president across the country.

  2. Ngakhale osauka titapondereza nkumaoneka ngati tilibe otiimilira koma ndi chikhulupiliro otiimilira alipo ndipo mlandu wa izi tikuchitudwa panozi mulandu wake ulipo no lawyer will be required .Everlasting punishment iz waiting

  3. Very funny while Rwanda is setting records of largest solar project, Malawi is setting its own damn records
    1-Being world’s poorest country
    2- Having a government with a bunch of most corrupt leaders
    3- Having a government of professional liars.
    This isn’t politics, its foolishness of individuals!

  4. Nkhani Ya chimangayi ifera mmazira chifukwa chaponda ndi mutharika ndi ponda mpondepo ndi zoti akhoza kumangitsana aaa ai ndithu ndakaika ndithu!Anthuwa ali limodzi mpake akubisana,

  5. Nawonso a Lukasi Kondowe ku ACB nkhani ya a Chapondayo kufufuza mpaka chaka?chonsecho anzanu angofufuza mwezi umodzi basi.Kapena nanunso mukuopa kupangidwa chips ngati Issa Njaudyu!kkkkkk!Iyaaa! Nanga ukutani osamutsekela chapondayo?

    1. Iwe Lukas Kondowe,ngati ntchito yakukanika uchoke wamva?Usatitenge a malawi ngati zitsiru ai.Ndimakumvera pa zodiak pa TIUZENI ZOONA koma palibe chanzeru chomwe wayankhula kape iwe!Ngati umadana ndi deputy wako Reneck Matemba,ndiye amalawi ungawatumikire bwanji?chamba eti?Ukapanda kummanga chapondayo sumwa madzi mphwanga!

    2. Zikomo a Kondowe pa zomwe mwachita.Dzulo ndinakunyozani kwambiri chifukwa kwa ine palibe chomwe mumachita pa nkhani ya a chaponda.Pano akuti mwakalanda dzindalama kunyumba kwa a chaponda.Tiyeni nayeni ameneyo komaso Foster Mulumbe mummangenso galu ameneyo anabaso.Mukawafufuze abale akenso kumudzi kwao asakupusitseni ai.Pomaliza bwana pa ndalama za a Chapondawo mundiganizireko pang’ono chabe ndigule pepala nyumba yanga ikudontha kwambiri.zikomo Sir.Inunso mutengepo pang’ono mugule KAMBA wa ana kunyumba.Kkkkkk!

    1. Guys,ndaganiza mofatsa tsopano! 2019 tisankhe Kamulepo Kalua as president of Malawi chifukwa akudziwa njira zomwe a ndale amabera ndalama za boma.And iyeyu sadzabanso ai chifukwa anaba kale.kkkkkk! Nanga njirazo akuzidziwa bwanji?

  6. The alwes get a way of distinguish the fire…the evidence is gone.

Comments are closed.