Govt to construct stadiums in Ntcheu, Zomba

Advertisement
Goodall Gondwe

Malawi government through the Minister of Finance Goodall Gondwe has announced that government will construct stadiums in Zomba and Ntcheu.

Gondwe made the announcement during the mid-year budget review in Parliament.

“Expenditure on domestically funded projects has been revised upwards by 10.7 percent, from K38.6 billion to K42.7 billion, to finance the commencement of the construction of the Mombera University, some roads in the three cities, and stadiums in Ntcheu and Zomba,” said Gondwe.

The building of the new stadium in Ntcheu will be a relief to the people of the district as the only community stadium in the district was demolished and the land used for a bus depot.

In Zomba, it is coming at a time when Zomba community stadium is in a bad shape and not fit to host highly competitive games in Malawi.

Meanwhile, the government also has plans to renovate Kamuzu stadium.

Advertisement

137 Comments

  1. Ife tidzaimba nyimbo zotamanda ngati izi mukuwuwa zitathekadi osati pano kuti tivutike ndikuomba mmanja ndiye tiyamba kuombela mfiti mmanja ndikudziwa ndiyolowela mu 2019 akudziwa Ntcheu ndi zomba ndi yotengeka ndi mabodza

  2. Yes, Zomba needs a good stadium, but Ntcheu needs water, electricity, up to date hospital, nice schools and job creation first. Stadium later.

    1. Magesi afalikila pano zamadzizo ndi mbiri pano chipatala sinkhani coz even wakululongwe amapezeka ali ku Qech ena amapita ku SA,ENGLAND,INDIA nde mukukama zomwe kutchewu tinathana nazo kale. Ngat munapitako 2004 go today u will see de Difference including new Bus Depot

  3. Ku BK kuli stadium ku Dedza ilipo koma game nkumachita kusowa super leage ikayamba ndie enawo achani??????

  4. Thanks Govt For The Stadium In Ntcheu,after Turning Community Ground Into Bus Stage Pple Had Nowhere To Watch Local Football Especially At Boma,i Can’t Wait To See Beautiful Stadium At My Beloved District,WAWA angoni.

  5. Hahaha am concerned bra checkout this Boma is wack why u busy with ma Stadium ngati kulibe zina zofunika mpira Flames simatha sanawinepo what a fuck who’s bringing nonsess propositions aaaaa koma malawi ine va ziiiii Yjb Mkango

  6. What a joke! Osangonena kuti u want to build ground losewererapo mpira bwanji instead of kuzivutitsa kunena kuti u want to build stadium.

  7. this is a good development ,we need to invest in football if we want to achieve our dreams of winning, government congrats, maybe someone wanted to hear that the minister shall construct his house,shame, pliz government these are Malawians who opposes even kokanyera munthu ukafuna kupita, its nonesense complaining tingoluza maflames coz sitinapange invest yet apa mususa, MUFUNA AKAWAKE MANDA AAMBUYANU CHANI? NDATOPA KUMANGOSUSA ZILIZONSE, UFITI, MAJINI, CHANI?

  8. The govt won’t be distracted with frivolous assertions. The country is fast moving forward. Slowly Malawi is changing for the better.

  9. Kodi inu a boma ndinu makape eti tionana 2018 koma mukuona achinyamata mu matowunimu ndi mamidzi muli anthu akusowa kenakake koti angayambile business koma ndalama mungothera zopusazo mukamanga ma stadium anuo anthu opanda ndalama adzikalipila dothi mungokula mitu osamaganiza bwanji ndalamazo kubweleketsa kwa achinyamata kuti ayambe ma business ang’ono ang’ono ai nthawi yanu

  10. I heard the minister of finance talking, he listed a number of projects which included the construction of Mombera university, Mzuzu airport, Zomba stadium, Ntcheu stadium just to menrion but a few.He said these will start soon using the 2016/17 budget.Malawi24 just heard of two stadiums.They could hv called the minister to cross check info. b4 giving us.

    1. Waakulu awatu sanaphunzire utolankhani nde sangakwanitse kuyankhula ndi minister iwo kwawo ndikumvera anzawo akamayankhula ndi minister iwo nkulemba third hand information

  11. hello friends my name is Lucy Kalonga doctor abumen help me to cure my HIV/AIDS virus with an herbal medicine, am sharing this to the world to save some lives, believe me there is a cure, you can contact dr abumen on his email address [email protected] and you can also call or whatsapp his number which is {+2347085071418} please share to save lives.

  12. Northerners we are own our own no one think or cares about us like we are not even Malawians but we also contributes alot through tax payers we are not included on their budgets this is not fair just look at Mzuzu stadium so pathetic

    1. Did you hear the minister of finance well? He talked of Mombera university and Mzuzu airport among other things to be done in the north.May be we hv another Mzuzu and Mombera in the south and central

    2. Northen is not yet developed,mz city kumaoneka ngati ka mtsika…..like serious?????? Always south.i only see reserve bank to be the only viable devlpt in north.what else??

    3. Even asatipatse stadium ndiyachani tidya mpira ife va ziiii they are lot of staff we need ,more graduates still unemployed , what have they done to empower the youth we struggling everyday , whats sports after all malawi sizafika on map with soccer but corruption we in top 5 rank

  13. Awelcome Move indeed, these will be tangible developments of which pple will point even after ur regime.Ndizimene tikufuna zimezo abwana President. Big up !

  14. Guyz tisamango comenta zopanda zeru, mumthu wapatsidwa kanthu kwake mkulandila osatiso aganizire za mavuto akomwe kukuchokera thandizolo. zikakhala za mavuto ndi zawo kudzabweraso boma lina adzakhala ndi mavuto awo.

  15. Ndalama za ma stadium zapeka? zolipira aphunzitsi zimasowa? mwezi wasala pang’ono kutha uwu mudikira akapange ma demo ndiye muwapatse ndalama zawo? mwatikwanatu.

  16. ntcheu akunenayo chanzeru ndi chimene chimamveka ndi ka private school basi or taxie rank kulibe, kanseu mkamodzi kongodutsa pa bomapo munthu umangozindikila akuwuza kuti tadutsa pa ntcheu boma… very poor servise delivery.

    1. Ukunama iwe ku ntcheu madzi ndi bweeeee ma school ukukambawo nde mngosayamba zachipatala sumapita cha m’boma lanu lokha even aku Blantyre amapita ku Kamuzu Hospa so What ukukamba chani tax rank izabwera after stadium-yo iwe kwanu mkuuuuu?????? Ngati kuli maboma abwino mMalawi muno lina ndi NTCHEU wava.

  17. HA! I don’t think construction of stadium can improve our economy. I would advise government to priotise industrialisation. Imagine we do import everything including tooth peak. Do we anticipate economic improvement with this?
    That’s why I prefer professor John Chisi of umodzi party, he can speak my opinion

  18. Stadiums ???
    When our roads continue claiming lives ?
    It’s high time the M1 needs an upgrade probably to a dual courage level.

  19. Mumange ma stadium eni eni oti nthawi ina mkudza African cup of nations osati tima stadium mupite ku Gabon mukaone ma stadium

  20. Muzipanga zomwe mwaganizazo, osati mutigwire m’maso ngati pomwe mumaba ndalama cmanga munatiuza poti njira zanu zobera ndalama ndizimenezo koma tidzaonana po VOTA mu 2019kkkkkkkk

  21. Malawi sazatheka ndipo ndife ochuluka nzelu.team yamalawi ikaluza mumati kumalawi kulibe zipangizo zabwino kumbali yampira wamiyendo ndipo choyamba mumanena ma stadium.lero akuti boma limange mastadium awiri mwayamba kuchuluka nzelu. malawi tinachenjela mopusa. malawi zuka! ukugonabe kunja kwacha tsopano.

  22. boma lili ndrama moti singalephele kumanga stadium ndi zitukuko zina nthawi yimodzi, komano mastadium azikhala owoneka bwino moti zaka zikubwelazi tingazapange host african cup of nation

  23. ma project enawa ndinjira chabe yoti abereko ndalama pali nzeru panyumba pali njala mukugona mopanda magetsi mulibe or mjigo wa madzi basi akukagula pool table muzisewerapo panyumba, umangozwirathu bambo mawaya ayamba kutaya mmutu

  24. Boma lathuli silolephela koma fundo zmapelekedwa kumeneku ndzo zkuchitsa bomali kuonekela kulephela,kkkk amalawi mpila unatphonya unless atherwise tkonze kaye stadium ya Blantyre

  25. How interesting! If the minister did his home work he might have realized that people from Ntcheu do not need a stadium the most. They need water, electricity, hospital facilities with medicine in them. What is wrong with our leaders? Malawi @53 still has no running water in many districts. Our hospitals in a very depleted state.

  26. Ikani Phula Mseu Wa Phindu Kwambili Pamtuteni Ochokela Kukatuli Kupita Ku Mangochi Osati Kwa Akabudula Kopanda Phinduko Ayi

  27. Electricity & water first, we r still drinking untreated water from the rivers, lakes & wells, n magetsi komanso miseu yabwino ikakhalapo ndi imene imaitana chitukuko mdera, u must ask the owners of this nation poor malawianz about what we need most, don’t dream yourselves n Kukwanirisa maloto anuwo

  28. Mangani nseu wa Zomba chitakale via phalombe,Phalombe hosp Kaye then mudzimanga ma stadiumuwo.
    When are you opening MJ stadium,ma china adamaliza kale

  29. In this damned-country,the priorities are always upside down…..Hospitals…Schools (Tertially going dwn)..Agriculture(Statins,,,etc) are very Poor,,,No maintenanc/Upgrade…not even an investment…..amangodziwa kupala Miseu bax, then aziti Development………Ndee akuona ngat ifeo tizizadya ma stadiums-wo?

  30. Mmmmhh ku Ntcheu munayamba kalekale kumango promiser zithu koma osakwanilitsa dele mmene mwayamba chonchimu ndkufuna kunyengelel mavoti bc munayambila bodza lanu pa mseu wa tsangano kut mumanga kom mpaka lero so pezan ina zokamba kuno ai

  31. i think there are a lot of development projects which the government can do instead of wasting money on stadiums. afterall mpira timangoluza. or else ndalamazo angogawa kwa anthu ovutika they will be blessed than the stadiums.

  32. Its very strange to me that this is being annonced by Ministry of Finance. Where is the responsible ministry for this? This is exactly how corruption finds its way into gvt departments.

  33. I’m not against this development, but the govt should try to priotise general welfare of Malawians. We are in great need of quality water, electricity and food, try to priotise these things first!!!.!

    1. Those projects are already priotised,u miss the outlined number of projects that the govt is implementing eg kamwamba coal powered electricity.mulanje mountain and lake malawi water projects.

Comments are closed.