Mafumu akufuna amayi aziloledwa kuchotsa mimba – atelo a Lukwa

Advertisement
Man impregnates his sister; says they are in love
Senior Chief Lukwa of Kasungu
Mfumu Lukwa akuti mafumu ali mbali yoti azimayi aiztaya pakati.

Anthu a mipingo ndi ena onse amene akudana ndi lamulo loti amayi aziloledwa kuchotsa pakati asayese Mafumu ali mbali yawo.

Malingana ndi Mfumu Yaikulu Lukwa ya a Chewa, Mafumu akugwilizana ndi lamulo loti amayi aziloledwa kuchotsa pakati.

A Lukwa amene ndi mlembi wamkulu wa bungwe la Mafumu ati iwo monga Mafumu ali okonzeka kuchita zionetselo ngati aphungu akane kukambilana za lamulo limeneli.

“Takonzeka kuvala mikanjo yathu ya ulemelero ndi kupita ku nyumba ya malamulo komweko kukawauza a phungu kuti nkhani imeneyi tikufuna ikambidwe,” anatelo a Lukwa.

Iwo anaonjezelapo kunena kuti Anthu amene akudana ndi lamulo lochotsa pakati sanakhale ndi nthawi yowelenga zimene lamulo limeneli likukamba.

“Nkhaniyi ena angoyankhula mwaphuma, sanawelenge za lamulo limeneli ndi komwe. Anthu otelewa asatisokoneze,” anaonjezelapo.

Lamulo lovomela amayi kuchotsa pakati linakolela moto pakatipa a mipingo atachita chionetselo chokana kuti pakhazikitsidwe lamuloli.

Advertisement

312 Comments

  1. Musatiwawitse mutu ndi nkhani za nkutu ngati imeneyi mamfumu sakudziwa kuti kodi kuseli kwa mchitidwe umenewu kuli chani akapatsidwa timalawasi basi asintha zolankhula.stupid

  2. Zaugaru Akufuna Kuti Azimayi Athu Azifa Pamodzi Ndi Zimu Wamwanayo Kd Yiyeyo Fumuyo Akanaramurira Athu Ake Akanachotsa Mimba Amake Kupusa Aziuza Ana Azichemwari Ake

  3. Akupangazo ndizachamba, Mulungu anati, tibelekane tichulukane ndipo tiligonjetse dziko lapasi, ndie zimenezozo kumbali yanga sindikugwilizana nazo

  4. Pepani amfumu ngati uli ufiti, kapena u hawe pachitumbuka, kapena usawi pa Chiyawo, mwaonjeza, muli ndi udindo ngati mfumu kulimbikitsa amayi apakati kuti azidya mokwanira kuti mwana alimmimbayo akhale wa mphamvu, koma inu mkuwalimbikisa kuti azipha, zedi amfumu? Mwina mukufuna timichombo??

  5. Kuchotsa mimba ndi kupha.

    Mimba ndi chipatso cha kukondana komwe kumachitika m’banja.

    Chiwerewere chimankhala tchimo (chigololo) chikamachitika pakati pa anthu awiri omwe saali pabanja.

    Kuchotsa mimba ndi kuchimwa kawiri kwa anthu amene achita (chigololo)

    Kuloredza kuchotsa mimba ndi kukanika kuletsa anthu kumvera Mulungu lamulo lake losachita chiwerewere musali pabanja kuli kusefukira kwa utchisi.

    NOW READ THE WORD STRAIGHT FROM GOD HIMSELF NOT THROUGH HIS MESSENGERS!!! Bible Verse:…. Deuteronomy Chapter 28 Verses 1 to Chapter 31.
    “If my people, who are called by my name, humble themselves, ………to do my commandments (which include Not to do Adultery) …….

    Mafumu mumudziwe Mulungu wamakamu kuopsya kwake. Sikuti nonsenu ndi agule wamkulu kuti simumudziwa JEHOVAH WAMAKAMU mphamvu zake.

    Pajatu mntundu waanthu ukachimwira JEHOVAH, mngakhale nthaka, agalu, nkhuku, mitengo, currency, morality, mvula imene zimalawa nawo mnkwiyo wake.

    TAKE CARE MAFUMU musadatokosole mnkwiyo wa OLENGA DZUWA.

  6. After all who is Mfumu Lukwa to mislead as? Just bcoz is called Mfumu ndiye tizingonvera ndi za nonsese zomwe? Mwazolowera inu kupangira business miyoyo yathu. Kwagwere uko ndi ufumu wakowo

  7. mpasu got arrested not that he stole money but there was corruption in the process of purchasing education material so why chaponda can’t be prosecuted for maizegate

  8. Mfumu yopanda mnzeru yosaopa MULUNGU, mudzi wakowo ukanakhala wopanda anthu ukanatchedwa mfumu?? Ufiti wakowo kumudzi kwanu konko!!! Wanva … Umalankhula kt akutame ndani¿? Ndi nzeru zako zopusazo. Uzimvere chisoni

  9. Mbuli ya munthu, kuteloku amabungwe aja azera mwa iyeyu. Mwalemba m’madzi never happen ngat afuna iyeyo ana ake azitero ife ang’eke.

  10. Aziyamba ndiwowa mafumu kutaya pakatiko. Why men are busy pushing to legalise abortions? Did they consulted women the pregnancy bearers or they just have thought it by themselves to push for it so that issues of wreckless impregnation takes its course in future? This is no bho mafumu sayenera kutero iwowa ndi ma custodian of our culture not to support destructive cultures of foreign men of underworld.

  11. amfumu inu mwapenga? kapena mwatan? zikanakha choncho mukanabadwa? nanga ufumu wanuwo bwenzi mukulamula ndani? mumadya fodya? ndkanakonda mukanandiyakha apo ayi ngati ndakunyasani mungondiloza mutchuke ndi inu.

  12. Mimbayo akanachosa amayawo iwowo asanabadwe bwenzi akuyankhula ali kuti?chifukwa chakuti iwowo anabadwa ndiye atinyase.Azimayi kumbukirani kuchosa mimba ndikuchimwa pamaso pa Mulungu.

  13. Kodi mafumu akungotengeka zilizonse bwanji? moti iwo saziwa kuti kuchotsa mimba, ndi chimodzimodzi kupha. Komweso kuli kuchimwa pamaso pa mulungu. Mfumu yosasamara moyo wa azimayi ngati imeyi. Mbuzi ya munthu. Umbuli omwewo kukulamuliran amfumu zoona! Ndakwiya nanu kwabasi. Muyenera mubwererenso ku school za kwacha.

  14. anthu.amene.anathama.ngamisala.ndikutha.misalayo.ndiku.marowa.ufumu.ndiye nga.amene.zachamba.bas.osata.mimba.yakazako.bwanji.sisisiiii.

  15. Ndichifukwa anthu akuti ziko lathu tsopano Satana akukulira kulirabe.Dzikoli ndilosauka kale ndiyenso tikuputa mkwiyo waCHAUTA pakukuyenda bwino?.Mafumu ngati mwasowa chochita museke pakamwa panupo,kodi kupanda anthu unu mukhalanso mafumu?.Mfumu amene wanena zimenezi amangidwe chifukwa ndikupha kumeneku,komanso ngati kwaiyeyo ili njira yabwino imeneyi: ayambe iye kupha ana ake onse anthu akuona kenakono anthu ayambepo kutaya Mimba.Mfumu yopusa kodi ndikusauka kapena ufiti?.

  16. Naa mayi olingalira bwino sangachosese mimba chifukwa akuziwa kuti kuchosa mimba ndi tchimo chifukwa wina aliyense akamapanga zimene amaziwa zosatira zake ndiye ngati usakufuna kutenga mimba kulibwino kumangopewa chigololocho chifukwa ndiye tchimo limeneliso lafika poyipa dziko lathu lino

  17. I Wonder How Relevant These Cartoons We Call Chiefs Are To The Development Of Human Values In Malawi? They Are A Total Waste Of Space- I Wish The Country Aborted Them Instead Of Aborting Innocent Babies!!!

  18. Ankanfunse Dan-Lu kuti mimbatimachotsa?Fumu yopanda nzelu imeneyi siyomwenso ilikumbuyo kwambava yotentha ma file a maize Gate xuiiiiiiii!!!

  19. Oyambe ndi mwana wawo bwanji. Ufumu wakewo ngotani mukuti olukwawo.

    Osamaone ngati Ochewa timakogdwa omachita iwowazi. Omewa omapembedza Mulungu uti kodi?

    Olukwa msatengeke ni onthu o ndale, tsatani chikhalibwe chanu tele!!!!!!

  20. Kodi lukwa ndindani?who is lukwa?very stupid &fuck you nonses,mafumu ake ati anenanawo zimenezo? Shit lukwa you decieve yourself &fuck you!

  21. Zopusa zaimenezo akanakhala agogo ako anachosa pakati abambo ako akanabadwa?.Ngati uli ufiti munene .ayambe ndi akadzi ako iwe lukwa

  22. Papa Lukwa lamulo limeneri akanavomera a Lukwa oyambirilawo inu nkukhala mgulu lochosedwa mukanauziwa kodi Ufumu wa dziko la pansi mukutumbwa nao lerowu … ???//??? Shame on u … !!!!

  23. Ndipo poti wanena kuti ndimfumu ya achewa koma akangokhala ndimisala ndikubwela kuno kumwela azaonachimene chidameta nganga mpala lizamuthela ziko komkuno ndipo uziti mafumu anyau osati mafumu akuno kumangochi fack you mind like animals

  24. mfumu yokonda ndalama tingopempha wamwambayo kuti akukhululukireni mfumu co simudziwa chimene mukupanga?{mwakutidwa ndimphavu za satana dyerekezi}

  25. Ku chotsa mimba ndi kupha komwe,ndie popeza iyeyi akugwirixana Nazo ayambe iyeyo kuchotsedwa,chitsilu cha munthu,ana NDA tsogolereri amawa,ngati anthu achuluka kuli bwino kuchotsa akalewo opanda nzeru komaso mbuli ngati zimenezi,akupatsaniko ndalama za maize gate zo eti, munthu ukakhuta umapita ku chimbudxi kukakhuthula ngati mwakhuta go to the toilet rather than coming here talking za uchitsiru.

  26. Yesu akabwera akuwona ngati adzakhala mpaka mpaka makape panonso mamfumu anatha angokhala mayina chabe komweko mimba imabwera yokha ? Ngati sunakozekele anakugwiririla ? Mwakhuta basi tichotse mimba tiyamba tachotsa inuyo inabwera. Asanakozekere amayi anu kuti berekela anthu opanda nzeru ngati inu ndinu ndani kuchintha zimmene mulungu anakoza ngati uli ndi ana akazi okha okha basi tsakulani. Ma Bar kkkkkkkkkkkk

  27. Lukwa Lukwa iwe, koma uli ndi ubongo? Mafumu ake ati? Lamulo lake liti? Umadya matewera a ana? a Lukwa a Lukwa… allow only women within your chieftainship tione ngati uzakhale ndi bumba in few years to come, kupusa! Chitsiru chimati mumtima kulibe Mulungu, oti kulibe Mulungu amati azimayi azichotsa pathupi, ….. Mukufuna kutinyazitsa a chewa bambo, ngati mwalandira chithumba from those pushing for the law, ingodyani bambo, mukutiboola m’makutu ife

  28. Mamfumu ena zitssiru akuoneka ngat azeru kufuna kukhala mbali yaboma kut alandre zambiri mfumu yopanda nzeru chitsiru mfumu imeneyi

  29. Mafumu ake aboma lakwanu fokolo ndipo kuno ku Nkhotakota tiwathyola miyendo akayerekeza kubwera nditifundo tawo tamakoponi fiti ua chabechabe imeneyi

  30. Kumbukirani tsiku lomwe muzakhala muli kunfunsidwa ndi angelo odziwa ntchito yawo kuti, kodi munkachotseranji mzimu wamunthu? Ndipo kaya muzakhala ndimayankho koma dziwani kuti mayankho anuwo sazaphula kanthu.

  31. Kodi nawo mafumu ake atiwo omwe akulamula zombwambwanazo mfumu ndindaniso mesa ngati akufuna mesa aziwawuza azikazi awowo kuti azichotsa mimbayo ndiposo iwowo akulamula ngati zikanakhala zimenezo ndeno iwowo akanabadwa mafumu mwandikwiyitsa kwambili ndipo achitsilu apresident kumangolamulila zilizose usilu okhaokha basi koma choti mudziwe chawuta akuyang’ana zonsezo ndipo chauta akulangani muwona ndipo azakulangana

  32. Kodi inu mazifum akadankhala azimanu adakuvulani ndi kukutayani mchi mbudzi bwezi mulipó munganize bwino osati mopusa ndinu opusa

  33. Kamfumu kopanda dzeru n pot peter mthalika anangokula mutu dzeru alibe dat y ali phwi mu ofece kukhalira kudya zigege pamoz nd lukwa wakeyo mafumu otero ndkanakhala ine kut ndkulamula dzikoli ndkangotuma ma bombocrat akangomotchera munyumba n kupasa ufum nd munthu oti dzeru alibe n iwe lukwa ngat ukuona kut ufumu ukfuna ukhalepo wekha chosesa mimba imene mkaz wako ali nayo!!!!!!! Ndwexo kape n ndangokuklangiza usabwere kuno usiku ndzakhala ndtagona ndaona ngat magaz a anthu akukuyenda kumaso coz unazolowera kumpha !!!!!ufit bas

  34. Ngati kuli munthu wopenga, gulukunyinda, mende, kwidemtete, ndi lukwa. Muli yamunthu. A P M naenso kupepera ndikumamva zokamba zambuzi izi, lundu, lukwa. Iti nditiwanthu tokonda katangale maningi

  35. Mafumu osaganiza ndamene akumakamba khani ngati zimenezi .akumaiwala kumene anachoka .akula afuna anonge malawi watsapoyi

  36. Lukwayo ndi mfumu lero chifukwa choti mai ake sanachotse mimba yomwe munthu wake ndi iyeyo. Bakili (Atcheya)paja adati:munthu amatha kukhala wankulu koma alibe nzeru.

  37. Mbuzi ya mfumu azichota akazako ndi ana aki ndi xi dzukulu zako anakakhala kuti amayi ako anachosa mimba yako bwezi uli mfumu iweyo

  38. Mfumu iyi imakamba zofoila nthawi zonse. Palibe chanzeru chomwe inakambapo ever since. Useless chief

  39. Kodi a Lukwa mikanjo ya ulemelero mukunenayo ndiye yoti? Makape inu mukanabadwa amanu akanachotsa mimba?

  40. Iweyo mfumuwe akadakhala kt amako adataya mimba yako lweo bwenzi pano uli mfumu?aaaaa,alukwa mwaganiza mopusatu bwino munyonzetsa nazomafumu amnzanu

  41. Walandila banzi ameneyi amuuze mwana wake zimenezo mfumu yanji yophunzitsa anthu ake zopusa Ndikukuuza iwe Mfumu Lukwa udzafa ifa yowawa ukangolengeza kwa anthu ako zochotsa mimba udzafa ifa yowawa

  42. Inkosi #Lukwa, where will you get mbumba if women are allowed to do it any how?? “i can only support maganizowa ngati pokhapo ngati mimbayo mkazi watengera pa ntchire ndipo ikusowa bambo polingalira chisamaliro cha mwana odzabadwayo”. kapenanso ngati mayi wamimbayo ali pa chiopsezo cha moyo wake apo mpo ee!!! not any how as this will increase chiwerewere malpractises.

  43. Ngati kuli Chitsilu China chamfumu nde ndi lukwa ndipo ngati samatamba ameneyu mmmm Matewela amadya ndithu, iweyo amai ako akadachotsa mimba yako ukanakhala ndi Moyo iwe ? chitsilu cha munthu iwe ndipo ngati ukufuna kuti azimayi azichotsa mimba iweyo uzilamulila chani kapena sumadziwa kuti dziko ndi anthu? Kopeka NDA Satanic anzakowo chitsulu iwe

  44. Kuzolowela ufiti samapephela amenewo musachotsele kapena kuphatikiza zolembebwa mu baibulo if mumapephela simudakalakhula zozelezeka ngati izi Malawi ndidziko loopa Mulungu osati munthu noted

  45. Tivote basi, kumvera mfumu kapena azibusa! Ine ndayambapo, mafumu olo kuwafunsa malamulo khumi a mulungu sakuyankhani, that’s y amati umfiti kulibe whay! Ali momo , ndavota pamenepo. Kikikiki

  46. paja timafumu tambiri ntima hule tinazolowera kunyenga tiana cholinga mukatipasa mimba tianato muzikachosesa muzikati ndi ufulu zopusa basi mesa kukhala mfumu ndi chambumba kodi ndiye azichemwali anu akachosa zimimbazo lnu mungakhale ndimbumba uhule basi

  47. Alukwa Bvuto lanu ndichani,,,,,,, inutu ngati mwadya zambili za dpp zikupangitsani kuti umfumu ukukanikeni kuyendetsa za ndale zikuphweteseni

  48. Kupus ngati msima mfumu yombwambwana koposa. Ufulu wanji otukwanatnkunyoza Mulungu uwu? Uwauze ana ako kapena zidzukulu zako zidzitero ndipo tizaotcha moto mukasewera. Ungalamulire dzikowe? Matambala mwadyawo akuphetsani nthawi isanakwane

  49. U chiefs, wat if ur mam had aborted u, wud u exists/?? Mafumu nonse mukuvomereza izi go to hell before we force you ourselves!;!!!!!!!!!!!

  50. Ma Ngos kaya mafumu noxe in support of this satanic point mimba zanu…funso langa ndi lakuti kodi anthu azipitabe ma church kumakapemphera kwa ma prophet kukafuna mphatso yamchibelekero atachotsa mimba 15 pa zaka 20??

  51. Ichi ndichifuniro chakumidima izi zikavomerezeka ndekuti maiko azungu akondwera koopsa,,,,mkazi akamachotsa mimba magaziwo azitengedwa mmphamvu zamasenga nkumakathira nsembe kumalo osutsana ndimlengi ndati zikangotheka posachedwapa mumva ma redio akusokosa ma donors apereka ma million mwakuti kudziko la Malawi,,,,,chithandizo chakenso chothera kumipando!!
    Ambuye atithangatire

    1. Iwe Sukunama, Olo Kansa Yamuchibelekeloyi Ngati Yiliyachilengedwe Ndakayika,akachosamo Zibelelozo ena alinazo buznec,ndiye Alukwa Andinyasapo Apa.

  52. Mafumu nde chaniso zianthu zosazindikila kumangodalira zisamba basi mbuli zenizeni mmufunse mfumu Lukwa kuti zikanakhala bwanji iyeyo mayi wakeyo akanachosa mimba ya iye? Akanaupeza ufumuwo? Zausilu basi?

  53. uchitsilu wa mfumu mwina naweso wadya chibaz panya pakopo galu iwe mwina ukuyankhulila kumbuyo ukamuuze mukaz wako wava chitsiluwe galu yo weta iyi isaa

  54. Mafumu onse adziko la pansi pano alephera,Tiyeni tidikilire ufumu uwu ukupezeka pa Daniel 4:34 . Pakuti mafumu apansi pano akuchita zomwe Zinanenedwa ndi Mlaliki 8:9

  55. Had It Been That Ur Mother Aborted U, Would U Be Achief Today? Think Before U Say Abortion Is Killing, God Will Punish U If U Dont Care.

  56. Ngayi kuli mfumu imodzi yopusa ndiye lukwayo ndipo amene anabvomeleza like a ameneyu kuti akhale mfumu ndi afiti anzako caus mayi wako amachotsa mimba yaiweyo maganizo opanda mzeruwa bwenzi ukulankhulira kuti kuzolowera nyawu kapena ndipo anthu akwalukwa m ulibe mfumu koma chigawenga Chopha anthu musamale

  57. mfumu lukwa inu mukanakhala mfumu popanda anthu ? ganizani bwino musalowe ndale ndinu mfumu yawanthu taganizani bwino

  58. Lukwa, ndiwe mbuz ndipo ndikutembelela kwa omwe anakusankha kt ukhale mfumu, kd mayi ako akanachosa mimba iwe ukanakhala mfumu? ndiwe opusa kwambili

  59. Mmm! Inunso a MALAWI 24 Musanyozetse mafumu anzeru apa amenewo ndi maganizo a # Denis Lukwa ka GVH Ka pa ntcheu akufuna akazi akewo azichotsa mimba atopa ndi kubereka ana onyasa.

  60. Afumu Lukwa its better for u if get tired ndi ufumu to handover the position to your nephew’s ngat nkumkwima mu obongo zitayeni izi .

  61. munthu opanda umunthu iwe subelekaso iwe, usatipatse tchito,fumu ya n’tundu wanji iwe,napankhani imeneyi yandinyasa kwambiriii.Munthu wa mutu kumiyendo,galu,mphaka kalikukutu,mphevu,koma iweeee!!!eee.

  62. Mafumu amene akusokoneza ulamuliro wa dzikoli nawa: Lukwa, lundu, Kaomba ndi Kyungu. They think they are the most civilised chiefs in the country kkkkkkkkk?

    1. Awa simafumu koma andale,kawirikawiri akupanga zinthu zautsiru,ngati azimayi azichotsa mimba ndiye anthu achuluka bwanji pamudzi?mfumu ndi anthu,sungakhare mfumu popanda anthu,

  63. I am from Canada I don’t understand your language. But APA mafumu apenga misala. Zoona mafumu akufuna ana osalakwa azipedwa. Anywhere admin I like your handwriting keep it up

    1. Kkkk. Ndimayesa fumu ndianthu, nanga mafumu akati ana ammimba aphedwe nanga ufumu wawo upita mtsogolo. Nanga Iwo mafumu akhala mafumu azinyama zakutsire. That’s why I am a virgin and I will die a virgin to set a good example to my kids

  64. mafumu adyera aku Malawi,wopusa ombwambwana mfumu yochititsa manyaz dziko lanulomwe kumamvera anthu obwera,amfumu inu mundisamale ndi mfundo zanu zopusa,adzipanga akazanu ndi ana anu zachambazo

  65. OSATI MAFUMU KOMA KUSERI KWAMA MFUMU KULI ATHU ENA AMENE AKUPANGISA NDE MUWONA KWIYO WA MULUNGU NGATI MA MP MUVOMELEZE KOMA ZIWANI ICHI MULUNGU SANGAKHALE OPUSA NDIKUKUPANGANI KUTI MUZIGONANA THEN KUTENGA MIMBA NDE NGATI MULORE ZIMENEZI MUSAFA IFA YOWAWA

  66. Mfumu yosaopa mulungu, kulimbikitsa mchitidwe wakupha ndakwiya nanu alukwa kooopsaa ngati ndiumphawi kaya zativuta

  67. Amai ambiri afera kufuna kumva chokoma. Iwo sadziwa kuti chigololo chosadziteteza munthu amatenga mimba. Inuso mukuvomelezanu amanu anakakuchotsani bwezi muli pamenepo. Uchembere wabwino sikuchotsa mimba, koma kudziwa njira zabwino zopewera mimba osati kupha ai.

  68. Mukamva mfumu ikutero mudziwe kuti ayifumbatitsa kenakake,mafumu athu ndi anthu opusa omwe amgwiritsidwa pazinthu zili zonse. Anthu akamagonana amadziwa kuti zotsatira zake ndi mimba,ndie muwalola bwanji kuti achotse? Mimba sibwera mwangozi kupatula ngati mkazi wachita kugwiriridwa.

  69. Apa timati monga mwadzina lawo loti amfumu lukwa,amfula,ufumu wawo ulibe zelu,kodi kupha ukuona ngati mkwabwino,mulungu amukhululukire ndithu zamanyazi.,,,shit!!!’,,,

  70. ufumuwakeuti ukumuyankhulisa mwapaujenipakewo, chisiluso chimenechi eti, boma lichitepokanthu ndithu apobi ndithananaye ndekha galuyo

  71. #_Lukwa i think you really dont know what you are tolking come on shame on you are you indeed a true king? watch your back please.

  72. Mfumuyo muyiwuze osamuke kumalawiko ikafune malo mayiko ena omwe angalole uchitsiruwo. Ndipo tiyambe ndi mfumu imeneyoyo Death penalty palibe angasekelere zopusazo

  73. ndipatseni nambala ya a Lukwa wo ndilankhule nawo.. iwo amayi awo anakawachotsa bwenzi akulankhura mopanda nzeru chonchi,, kodi munthu watenga yekha mimba, ayichotseranjinso? amene asafuna mimba akabaise kulera, osati kumatenga dala mimba nkumati mkachotsa , ayiiiii.

  74. Satana iwe!!!!! Ayambe amako kutaya mimba ya iwe. Ukuona ngati udagwa kumwamba eti. zoti iwe umavala ma tewela ndikumabibidwa ukuziwa? Ngati uli umphawi amalawi, Bola tingoyamba kugulitsa malitseche athu. tonse tokhale othena kuti mwina tikhale olemera komanso mimba zichepe kusiyana ndikumayikila kumbuyo mchitidwe onunkhawu. Ukutero akazako achitatu aja mimbayo achotsa liti???? Mxiiiiii!!! Ndakwiya nawe koopsa!!!

Comments are closed.