Police officer dies after taking herbs

Advertisement

A police officer has died after taking dangerous herbs in Nkhatabay district.

Reports that Malawi24 has gathered indicate that the deceased identified as Friday Kalonjere of Nkhatabay Police Station visited a herbalist together with his friend.

The two went to a herbalist known as Rabson Milanzi of Mongola village, Traditional Authority Nkanda in Mulanje district.

At the herbalist’s, they were given herbs but as soon as they took them the two began feeling unwell and when they left the herbalist’s premises the police officer began vomiting and collapsed instantly.

The two were rushed to the hospital where the police officer was pronounced dead before getting any treatment.

The other victim is still unconscious at the hospital.

Advertisement

42 Comments

  1. Mmm guyz aliyense ndi mtembo basi koma zimasiyana ndi nthawi,nde kumalankhula bwino msakhale ngati ndinu ambeu…..palibe angathawe imfa nde msachenjere pa imfa ya mnzanu chifukwa nanunso idzakuchenjererani,,,,,cmnts?al da best continue…

  2. Guyz musayakhule choch mwakula mwatha mawa ndnu mukanafusa kt makhwalawo anali achan osamangopang cmt zopusazo munazolowela kwanuko kukhwima zopusa nd mukuganizila izo azanut muzaziwona

  3. akuti munthuyu analedzera ndiye atafika pena pake anadzera kwa asing’anga komwe anakamupeza zake Akutenga mankhwala oti azithandizire mumimba koz iyeyo akapita kutoilet pamakhala povuta kut azitandize nde anangoganiza naye zomuuza sing’anga uja kut nane ndiliso ndi vuto ngati limenero mimba mwanga mungozaza nde mundithandizeko nane mwina kutheka zitha kukandithandiza , nde sing’anga uja sanachitile mwina ai koma kupereka mankhwalawo onse limodz ndi zake , koma atamwa mankhwala aja kuzayenda kamtunda pang’o wapoliceyu anayamba kusaza , zake ataona kut zavuta anamutengera kuchipatala koma asanafike kuchipatala wapoliceyu moyo wake unathera panjira koma mene amafika adotolo anawauza kut munthuyu wamwalira kale , koma xakeyo nayeso wagonekedwa ku chipatala konko

Comments are closed.