A Chakwera akufuna kulanda Boma – atelo a DPP

Advertisement
Lazarus Chakwera

A Lazarus Chakwera ndi kutheka anagonja pa zisankho mu 2014, koma a chipani cholamula cha DPP sakugona nawo tulo.

Malinga ndi chikalata chimene chipani cholamula cha DPP chatulutsa, mtsogoleri wotsutsa bomayu ati ali pa kalikiliki ofuna kuchita chipongwe Boma la DPP.

Lazarus Chakwera
Chakwera akuti akufuna kulanda boma malingana ndi chipani cha DPP.

Mlembi wamkulu wa chipani cha DPP, a Francis Mphepo, ati a Chakwera agwilizana ndi nyumba zina zoulutsa mawu mu dziko muno kuti azifalitsa nkhani zabodza ati cholinga anthu aukile Boma.

“Akufuna amemeze a Malawi kuti apite kumseu akayambe zipolowe,” alemba choncho a Mphepo.

A Mphepo ati a Chakwera ali pa kalikiliki olengeza nkhani yoti Boma la a Mutharika linachita katangale Pogula chimanga ku dziko la Zambia.

Ngakhale a chipani cha DPP akukana kuti sipanachitike katangale, ma report anasonyeza kuti kugula chimanga ku Zambia panayenda njomba.

Zinamveka kuti Boma linagula chimanga pa mtengo okwela kamba koti ndalama ina amafuna achite chosolola.

Pakadali pano, chimanga chikugulitsidwa pa mtengo wa K12,500 ku misika ya Admarc. Koma akuti chimanga bwenzi chikugulitsidwa pa mtengo wa K5000 kukanapanda kusololedwa.

Advertisement

281 Comments

  1. These DPP guys r talking rubbish ,just accept that u have failed to change the lives of Malawians not always shifting the blame ,leave chakwera alone just carry on stealing our money but be ready to face the law after 2019

  2. We’re looking for investors and first registered user who the whole Malawi will be under.
    Call/Whatsapp: +2348063160229
    Follow this link to join
    http://ultimatecycler.com/refx/signup/joshkeys

    YOU CAN ALSO JOIN OUR WHATSAPP GROUP NOW
    https://chat.whatsapp.com/D52cJjnvESPAfco96XGjXq

    Facebook Page
    https://www.facebook.com/ultimatecyclermalawi/
    Ultimate cycler has come to stay and make our life better

    Register with MK10,000 and get MK40,000

    How it works:
    Get 4 people and be paid MK40,000 as soon as possible
    Get 2 people and get paid MK40,000 in 1week

    Get nobody and get paid MK40,000 after 2weeks..

    (Computer automatically merges u with 4 people)

    Ultimate cycler…… The Real Deal……..I was doubting it before but now I am a witness….

    Don’t be left out in this move for the betterment of your life.

    Register with MK10,000 today and stand a chance of being MK2,560,000 million richer in less than 4 months.
    ===========≈=============
    You join free and pay $25 (MK10,000) to the person nominated in the matrix, normally your 2nd level up, and you will have a spot in their 2 X 2 matrix. That is the LEVEL 1.

    Get your 2, and your 2 get their 2 and those 4 people that landed on your pay line, your green zone pay you $25 X 4=$100 (MK40,000). Out of your profit, re-enter and follow your sponsor in his new matrix and pay the person 2 levels above you. As that matrix fills again with 6 people under you, you cycle the $100 (MK40,000) again, and again without limit, giving you $75 (MK30,000) profit each time you cycle.

    LEVEL 2
    You upgrade with $50 (MK20,000) out of your profits.
    It is also 2×2 matrix.
    As your downlines follow you, together with spillovers from your uplines, you cycle $50 x 4= $200 (MK80,000). Re-enter as you did in the $25 matrix. You keep profiting with the cycle of $200 over and over without limit, giving you $150 each time you cycle, which is MK60,000 net profit over and over and over again without end.

    LEVEL 3
    It is also a 2×2 matrix.
    In the same manner, you upgrade to this matrix with $100 (MK40,000).
    At this level you earned $100 x4 = $400 (MK160,000), giving you a net profit of MK120,000 over and over without end.

    LEVEL 4
    It is also a 2×2 matrix.
    In the same manner, you upgrade to this matrix with $200 (MWK80,000).
    At this level you earned $200 x4 = $800 (MK320,000), giving you a net profit of MK240,000 over and over without limit.

    LEVEL 5
    It is also a 2×2 matrix.
    In the same manner, you upgrade to this matrix with $400 (MK160,000).
    At this level you earned $400 x4 = $1,600 (MK640,000), giving you a net profit of MK480,000 over and over again without end.

    LEVEL 6
    It is also a 2×2 matrix.
    In the same manner, you upgrade to this matrix with $800 (MK320,000).
    At this level you earned $800 x4 = $3,200 (MK1,280,000), giving you a net profit of MK960,000 over and over without end as you keep on cycling. It’s noteworthy that all these business centers operate independent of another.

    LEVEL 7
    It is also a 2×2 matrix.
    In the same manner, you upgrade to this matrix with $1,600 (MK640,000).
    At this level you earned $1,600 x4 = $6,400 (MK,2,560,000), giving you a net profit of MK1,920,000 over and over without end as you keep on cycling. It’s noteworthy that all these business centers operate independent of another.

    EARNINGS SUMMARY:
    ========================
    STAGE 1.
    $100 (MK40,000)

    STAGE 2
    $200 (MK80,000)

    STAGE 3
    $400 (MK160,000)

    STAGE 4
    $800(MK320,000)

    STAGE 5
    $1,600 (MK640,000)

    STAGE 6
    $3,200 (MK1,280,000)

    STAGE 7
    $6,400 (MK2,560,000)

    Payments Can be done with:
    Bitcoin https://blockchain.info
    Local Bank, PayPal, Payza, Hand-To-Hand.

    Click to register
    http://ultimatecycler.com/refx/signup/joshkeys

  3. Inu mukakwera bus ndipo driver nkumayendetsa molakwika,anthu amayankhula kumene koma akamyendetsa bwino, anthu omwewo amakhala phe.Tatiuzani inu a dpp mukufuna anthu asayankhule pomwe zinthu sizikuyenda bwino?

  4. Kodi inu munthu akati adzudzule kuti mwaba ndalama za chimanga ku zambia mukuti akufuna kuti akulandeni boma kodi mukuwona kuti amalawi akusangalala ndi zauchitsiru mukuchitazi musiyeni chakwera amutuma ndi amalawi osawuka osati inuyo mbabvanu ayiii.

  5. Chakwera akufuna kulanda Boma – atelo a DPP By Mwayi Mkandawire January 13, 2017 19 People You Won’t Believe Actually Exist ? A Lazarus Chakwera ndi kutheka anagonja pa zisankho mu 2014, koma a chipani cholamula cha DPP sakugona nawo tulo.Malinga ndi chikalata chimene chipani cholamula cha DPP chatulutsa, mtsogoleri wotsutsa bomayu ati ali pa kalikiliki ofuna kuchita chipongwe Boma la DPP.Chakwera akuti akufuna kulanda boma malingana ndi chipani cha DPP.Mlembi wamkulu wa chipani cha DPP, a Francis Mphepo, ati a Chakwera agwilizana ndi nyumba zina zoulutsa mawu mu dziko muno kuti azifalitsa nkhani zabodza ati cholinga anthu aukile Boma. “Akufuna amemeze a Malawi kuti apite kumseu akayambe zipolowe,” alemba choncho a Mphepo.A Mphepo ati a Chakwera ali pa kalikiliki olengeza nkhani yoti Boma la a Mutharika linachita katangale Pogula chimanga ku dziko la Zambia.Ngakhale a chipani cha DPP akukana kuti sipanachitike katangale, ma report anasonyeza kuti kugula chimanga ku Zambia panayenda njomba.Zinamveka kuti Boma linagula chimanga pa mtengo okwela kamba koti ndalama ina amafuna achite chosolola.Pakadali pano, chimanga chikugulitsidwa pa mtengo wa K12,500 ku misika ya Admarc. Koma akuti chimanga bwenzi chikugulitsidwa pa mtengo wa K5000 kukanapanda kusololedwa.

  6. Ndikanakondwa ngatizitatheka achakwela kutenga dzikolo ndikuwasiyila bomalaolo dziko linawasankha Amutharika Amutharika anasankha anthu ndikupanga boma, ndikuma zumza dziko kuiwalakuti ndiosangidwa chomwe amakumbukila ndikusankha, osatikusankhidwa kwao anayila kuti ndiosankhidwa.

  7. Chakwera akaopedwe ngati chilipo cha nzeru chomwe akunena iye? Ndale zophunzirazo palibe chilipo cha nzeru ndipo sangawine amene uja. Angobwerera azikalalika uko.

  8. Boma salanda ngati akulanda chimanga chootcha zautsilu baxi,, mwayima nawo kangati pazisankho? Munayamba mwawinapo? Obvious mr APM dziko lamulephera koma tikufuna tifatse posankha munthu woti angazayetsese kuthetsa mabvuto athu” tikati mabvuto we mean kuchepatsa njala (1) chachiwiri malipiro komanso ntchito, jst imagine chimanga thumba likugulisidwa Mk12,500 instead of Mk5,000 what z that? Sono ngati inuyo Achakwera mungazakwanitse dzinthu ndanenapazi it’s fine u ar welcom koma musabwere poyera kumanena kuti mukufuna kulanda boma coz mukazaluza pamawa anthu azakusekani..

  9. A DPP akusakasaka njira zoti aperekere boma mmanja mwa a Chakwera iwo la wakanika. Masitha defecters mulimo m’Malawi muno? Mwanoti ziii.

  10. Bodza ilo alanda boma bwanji a Chakwera? Atakudzudzulani basi mwati afuna alande boma? Kuvomereza kuti mwalakwitsa ndi bwino. Sindilikukhulupirira kuti mutamachita bwino angamalankhuleso mwina zomwe zikukuphetekanizo, koma ngati simukukhoza akuyenera kulankhula. Ndiye nanga poti si a Chakwera okha alankhula, pali a mabungwe komaso a Malawi ambiri akulankhula, tinene kuti onsewa afuna kulanda boma? Ndiye ngati zilichoncho ndiye chokamoni n’bomamo kuti a Malawi eniake ayendetse dzikoli mwina chipani cha DPP ndi cha anthu akunja omwe sakudziwa kuti dzikoli lili ndi achiyeniake amene amalifunira zabwimo dzikoli. Osati kuponderedzana ngati zomwe tikuzionazi.

  11. Zitsiru zosowa fundo za kumwera zili busy zimvekere chakwera analephera kuyendetsa mpingo, komaso anaba za mpingo mulindiumboni? ati kufuna kumpezera zifukwa chakwera zazii, bibulo lake liti limeneli ?baibulo limati musawereluze ena, chiwerezo chili ndimwini wake mulungu.inu chakwera sioyamba kujoina ndale mwava? John chilembwe, Desmond Tutu wa Ku South Africa komaso papa tsogoleri wa roman Catholic amalowerera ndale.inuyo machimo alithoo koma busy kuwereza azanu .pathako pano nonse akumwera .

  12. U must always remember cash gate err that blave woman robbed money. When Mlomwe and his cabinet entered DPP anapeza mulibe ndalama.Olo mutachenjera maka simungasinthe zinthu.5years ngati mulibe capital, zimapepuka zikakhala kwanzako DPP boma.

  13. Don’t stop giving them pressure, 2019 election you will be President. See how they are losing by-elections. It will be in the same way.

  14. Wandale Aliyense Ndiwakuba Ngakhale Chakwela Akadzalowa boma
    Azaba Kwambiri Kuposa Peter Osakhulupilila Anthu Andale Ndipo Katangale Sadzatha Zapadziko Izi

  15. Wandale Aliyense Ndiwakuba Ngakhale Chakwela Akadzalowa boma
    Azaba Kwambiri Kuposa Peter Osakhulupilila Anthu Andale Ndipo Katangale Sadzatha Zapadziko Izi

  16. I have never seen boma la mantha like this one.Chakwera asatsokomole AAA iai afuna alande boma,asapite Ku maliro ayi wayamba kampeni iiiiii kma

  17. we dot want x 2 b presdnt but we nid changes so that we live haply.we dot hate apm nor dpp bt the way economy is.unless u tel us that things are ok,u cant tolerate it.may b problems rocking the country do not affect ppo who r strong dpp sapotaz.

  18. what I observed is that politicians are lyk football clubs officials,they only being angels on opposing once gven a chance of ruling nzeru zonsezija ng’ooo.

  19. Chakwera ndiye mbava yeniyeni.lnu anaona kuti chopereka Chimachepa ali koma ndikawone kundale.guy osachita mistake .Osaiwala anagwa MMANJA mwamulungu ndi jabulosi uyu mph wake wauja anaismpusisa Hava uja.

  20. Koma a DPP akudziwona uchisiru wawo, ayamba mantha tsopano akudziwa kuti Chakwera atenga boma pavute pasavute. Musanati DPP ndiya zisiru zokha zokha.

  21. Munasiya Ma Bible Ukooooo!!! Nde Lero Mwat Mupange Ndale!? Komwe Uliko Chakwera Umve Kut Mulungu Wakwiya Nawe Ndpo Boma Lino Sudzalamulira,pomaliza Mutu Wako

  22. If you didn’t vote for dpp you must just kip quite mkut dpp inabela mavotes pomwe ineyo ndnavotela dpp ife ambritu tinaivotela but the problem comes when you see that agalantia sanawine aliyese anavotela chakwera analuza sungamat ndewu ija sinaluze komano ndmangofuna mtendere that’s why ndavomeleza kuluza don’t lie to ppl when you luz u luz don’t expect to win when you gatta pikinin supporters DPP ND BOMA

  23. Mukumuopa Chakwera,Abusa sangalande boma,koma inu a Dpp zangokuvutani basi.osati mumupedzere zifukwa zoti mudzimumanga munthu wa a Mbuyeyi ayi.Musamusokonedze musiyeni munthuyi..

  24. Awa achakwera sangakhare papando komanso ndikaona mavuto akulu ndiakuti unsongoleli wakakamira kumwera dzikumanyasa chifukwa pa dzatenga nthawi kt udzafike Ku chingawo chapakati.kuti udzafike chingawo chapakaki ayembekedzere dzaka 27.kunsongoroku osati pano mukalambira popo achakwera pa otsawoo ndiye pando wanu.achakwera osati oramura dziko never.

  25. chakwela wafika ponyada! ganizo lake ndilofunadi kulamulira boma! koma ndikanakhala peter sindikadalora wotsutsa azinditcha “patient/,olephera/mbuli yophuzira’ ndithudi akadandiva!! kwa ine chakwela mchitsiru,galu wa munthu,bwanji safuna kuthandizapo ndi zelu zofuna kuthana ndi mavuto we’re facing,bwanji sathandizapo odwala azipatala,koma kunyoza basi! zauchitsiru basi!! nanuso amalawi24 simulemba nkhani yoyamikira munthu,koma zomwe wina wanyoza boma basi! why? even mundi blocky vuto mayazi koma nanuso mumachita zauchitsiru! ndikadakonda nanuso mutakhala gulu lotsekedwalo.ndamaliza!!

  26. Kapeni inantha kale inu achakwera cholinga chanu mukufuna mutinthamangisire anthu amene akutinthandidza osati kuwaunikira amalawi.mukudziwa kale tengo umene boma limangulira chimanga.ubuli achakwera nanu munali mutaba kale dzapingo.2019. Munsowa dzopangira kapeni ndalama.

  27. Cardiac arrest redeemed us from dictatorial evil Bingu, another cardiac arrest is very soon going to redeem us from these evil walking dpp leaders, God is not Peter Mutharika or Chaponda. Just wait, cardiac arrest is looming

  28. Ine ndikuonanso KT chakwela ndiye mbava yeniyeni inu taganizani mozama komanso yamban kupenya patali munthu kusiya kutumikila mulungu,kusiya nkhosa zamulungu ndikujoyina ndale ndiye mukuona kt ndichanzelu? Amalawi azanga mwatan?bola mbava zomwezi

    1. U who is savage, savage ndi iwe ndi chakwera wakoyo ,akanakhala ozindikira akanapanga mapulani oti azawine 2019 osati kulanda boma, mphwanga ukalimbana ndine ,uyithawa MALAWI.

  29. Matenda avutawa adafalisidwa ndi #MCP amene amaumiliza kugonana ndi aliyense pogwirisa mphamvu za chipani komanso #Chakwera analephela kusogolera mpingo ndi azasogolera dziko lake liti?

  30. Matenda avutawa adafalisidwa ndi #MCP amene amaumiliza kugonana ndi aliyense pogwirisa mphamvu za chipani komanso #Chakwera analephela kusogolera mpingo ndi azasogolera dziko lake liti?

  31. Matenda avutawa adafalisidwa ndi #MCP amene amaumiliza kugonana ndi aliyense pogwirisa mphamvu za chipani komanso #Chakwera analephela kusogolera mpingo ndi azasogolera dziko lake liti?

  32. Peter mutharika ndi proffesor wa mkalasi osati ku ndale,utsogoleri ndi mphatso yochoka kwa ambuye osati kungogwera ayi,munalowera pawindo lero mutulukiranso pa windo

  33. guys do your politics am never voting again,, to hell with malawian politics you make the country look stupid but God is watching you.

  34. Chakwera is a failure.who can put him on presidency. He failed to lead 200 people in his Church. No wonder he is failing to lead MCP .Lo a country; Malawi; with central region only. Forget .stop dreaming in vacuum.DPP woyee 2019 motomoto.

    1. you are a big failure too,more than wina aliyense,you a real blind bat,ndiwe cadet wa dpp eti,party full of madeya,zigawenga,mbava,mahule including u

  35. Osanama Boma Ili Latikwana Heve Angakhale Boma Ili Likudziwa Kuti 2019 Lili M’madzi Amalawi Onse Amadziwa Kuti Boma La Malawi Lidagula Chimanga Ku zambia Mwakuba Kusonyeza Kuti Chimanga Chomwe Chidabwela Kuchokela Ku Zambia Ndindalama Zomwe Boma Lamalawi Limanena Kuti Lidagwilitsa Tchito Sizimayenelana Ndalamazo Zimachuluka Pomwe Chimanga Ndi Chochepa A Cham’kwelawo Sakunama Boma Ili Linabadi Ndalama Za Mondokwa.

  36. Chakwera is the most stupid person in Malawi coz he failed to take the government through ballot paper. i Dont think he can take the government through any means. He must be kissing his anus……

    1. You are the most stupid and foul mouthed mbuzi on this page. Yea, like all dpp supporters. Always clapping hands for mediocrity

    2. mr jumbe u are also very stupid including your mother and father. i have believed that writing words like this is not good but this is being promoted by mcp supporters who are fond of insulting the leader of this country by doing this. lero tikamabweza muzikamba zambiri. Go and read what mcp supporters have written on this page. Tonsefe sife a mcp and mudziwe zimenezi. Inu a mcp mukatukwana ntsogoleri wathu wa dpp ifenso wanuyo tizimutukwana agalu inu.

  37. Ndimamva chisoni kuona anthu mukukangana nkhani zokhuza agalu andalewa taganiza ndi mtsogoleli uti yemwe analowa m’boma ali osauka ndikutulukamonso osauka? Ndiye muzifunse why, kapena chikuna ninji aphungu athu sanayambepo akana kuti musationjezere malipiro nthawi iwo tiyambe takonza za mavuto ali mdzikowa?

  38. Its a time for DPP to rule this country ngat muli ndi milandu khani ndi pa 2019 election bas ngat azalowe enawo tizaone ngat azathetse mavuto M’Malawi.

  39. Its a time for DPP to rule this country ngat muli ndi milandu khani ndi pa 2019 election bas ngat azalowe enawo tizaone ngat azathetse mavuto M’Malawi.

  40. Nkhani ya chakwera wanuo imandinyasa kwambiri anakanika kutumikira nkhosa zamulungu kuli bwanji kutumira dziko? Chimu2 chadyera ngati chimenechi ndipo akungovutika ndikubwebweta sangawine ataa!!

  41. O Ooooo Zamwe Mungandiuze Nthuni Inu Tsanotu M’mepa Nzongoonetselatu Kuti Ochakwela Oludzatenga Boma 2019 Komasotu Odara Ochakwela Sodaname Boma Iri Its Verry Hurd Kuba Odala Olutibela Olukapondeleza Kadziko Koomalawi Tsanotu M’mepa Okadapanda Kukhalako Mavenda M’mewa Dalatu Oma Admarc Om’mewa Okadati Gwirililatu Tikadasowa Kothawila Koma Oma Admarc Om’mewa Okhaula Ochimina Odziwaso Anya Awona.

  42. kawirikawiri munthu amadana ndi chilungamo. Aboma mulikuba koma musatiopseze ai. makamaka chaponda mbava aDPP nose shem. chakwela sakulakwa vuto ndinu. Zodiac sidalakwe akukamba zoona, boma lakuba shem!!

  43. Dziwani izi amalawi anzanga mungovutika ndikubwebweta za Galatiya uyu mukuti chakwerayu ameneyu oro zitavuta mpaka sangatenge boma la Malawi ndipo sadzalamulako mpaka kalekale ufuse John tembo bwino bwino .Amene adzalamule dziko Lima Ali pheeee inu simukudziwa munya muona tamangosililani ulamulilo wamzanuo ng,ooo

    1. uli mgulu loti people from other regions will not rule this country just wait and see how thing are turning out to be its not about comming from densely populated region but what you achieve for the majority remember what David did to Goliath

    2. kodi iwe freza mutu wako umayenda bwino despite it has no legs upite kumento ndakuuza kale chakwera ndi Galatia anayamba zabwino akutsilizila ndizoipa waba iba za mumpingo pano akufuna kudzabaso za boma la malawi komatu ayaluka

    3. thats de point man,idont think mcp will rull dis country again,zowona ndithu agalu a mcp kuthamangitsa azungu kenaka mkumawapemphaso,bwezipano malawi alipati

  44. JUST CHANGE UR STYLE OF LEADERSHIP,STOP OPPRESING THE POOR, DO WHAT IS RIGHT PALIBE AKUFUNA KULANDA BOMA APA PPLE WANTs JUSTICE TO PREVAIL WHY R YOU STIL KEEPING THAT TWO FINGER CHAPONDA?

  45. a Malawi panopa azindikira sazaperekanso zaka 10 kwa President kuti alamulire dzikoli,,,,ndi Bakiri yekha yemwe anakwanitsa zaka ten,,,Bingu zaka 8,,,anamuchotsa ndi Mulungu pa mpando a Malawi atakwiya ndi ulamuliro wake mu term yachiwiri,,,Joyce Banda zaka ziwiri nayenso atangotsegura loko anthu kunali kuba ndarama ku likulu la boma,,,anthu anakwiya naye ndipo sanamuvotere amene anajijilika kumuvotera ndi omutsatira akewo,,,ndye awanso a Petulowa mukumva kuti zachitika,,,,koma 2019 sadutsa

  46. Zoopsezana zidatha nthawi ya chipani chimodzi. What is wrong with the leader of opposition when he opposes? If ordinary citizens are opposing, what do you expect the “leader” of opposition to do? Do not think you will be there forever. TIME WILL TELL. Dphwiphwiii chipani cha mbava, zigawenga, the failures.

  47. Haha #Chakwela amphawi wamukwana bola dpp kaya mukut ndiakuba bola tizitukuko tao taziona olo atati achoke lero titha kuzilodza nanga Chakwela olo atati wafa lero muzaloza kut wakupangilani chan agalu inu? Mcp ndmaipasa ulemu ndkamamva za #Kamuzu osat ana onyela nyelawa aka #Chakwela zazi dikilan muonenso dpp ikuwinanso kachikena cz #pp inatha #udf inatha #Mcp akungokanganamo okha okha mpaka kuotchelana ma galimoto bcz of Chakwela ndye mukuona ngat Mcp ingalamulire dziko lino Kkkkk mudakalirabe pepan

    1. u should be talking of DPP vs MCP not Chakwera vs DPP rather pitala vs Chakwera, pitala wapanga chani choti tizamukumbukire?

    2. Tatchula zomwe wapanga mdala wako wopanda manoyu ali mboma tiloza bwanji za chakwera ngt analamulilapo, umbuli osamachita kudzitsatsa osamangokhala osapanga cmnt bwa,kkkkkk km enanu kuvetsa chson

    3. galu wamkulu ndiiweyo..Chakwera analamulira dziko lino liti kuti tikaloze chitukuko chake..Ibu wakoyo nde palibe 0 weniweni akungotisaukitsa ali pheee galu nzakoyo nonse ofunika chain

    4. Komaso bola nthawi ya MCP yo timazuzika mukutero koma cilicose pamoyo Wa munthu cinali bwino talk of cakudya ,maphuziro, umoyo, magetsi in short zonse zinkayenda nanga pano

    5. Haha ndzakupasan ulemu nonse amene mukunyoza dpp mukazafa ndiamene ndtazaziwe kut mdziko munodi mulinjara nanga munayambila kudandaula muja simukufa bwanj mpaka pano mulindizizukulu zanu enanu mpaka mwakula opanda chilema ndye mavuto ake ati mukuwanenawo zaulesi basi muzipanga maganju ngat ntchto zikusowa or mumuuze #Chakwela wanuyo akulemben ntchto yosesa zitosi za #tambala wakuda mumvekere kwacha ! Kwacha ! Ndye mukudandaulanji mesa kumalawi kwacha kod Kkk bravo mr #Peter #Muthalika ziko lilibwino kale ili but akufuna kusokoneza ndi awa a #Chakwela anathawa ku lalikila mu church pano akutukwana presidnt aneneri onyenga mumakwana mr ka Chakwela go to hello wif yo fuckn cheap pussy party well knwn as #mcp

  48. Driver akamyendesa basis mwausilu atha kuphetsa anthu,alandidwe stealing ena ayendetse anthu akhale moyo. Ah sinaone bama lonseli kukaopa munthu mmodzi. Nanga akazayamba ntchito limodzi ndi manganya si ma bp,ena kubibidwa ngati nthawi ya treason case ija.aaaa. mwinadi mavoti zisakho zapita zija kalipokalipo kanachitika kwa chakwera.nanga mantha amenewa bwanji anthu asyankhule basi mayooo mayooo.

  49. A malawi24 ndinu abodza munatinamiza kuti the president is going to conduct a rally in nsanje on wednesday apa mwanamanso i can see politicians driving u. Paja munthu akakutsutsani u brock him ngati afriem brock me.

  50. U are failing to get inner peace because of the maize u steal. For show you will lose come 2019.this is multiparty democratic nation. Why u always want to silence a potential party. We are sick of your games. Kachipani kaanthu akuba

  51. Nawo adpp ndi manyaka bwanji !! Wy kumalimbana ndimunthu oti he wont b president az long az our voting system will still b based on majority rule ? Kodi mesa dpp comes from komwe kuli ambiliko ?? Mlekeni azawine kumpoto ndi central kwakeko !! Kwawo kwa mcp dpp izizapeza mavoti koma iwowo kuno ndi zero chitsanzo ndizisankho zinacitika zama by election Ku mcinji zomba kasungu pomwe dpp yapeza kukasungu pomwe kuzomba mcp zero . The same with mayor elections !!

    1. Tizakhumudwa Ku central region kwanuko !! More over Ife adpp sitikhumudwa but u & u always cry kuti mwabeledwa . Do u think kuti southern will overwhelmengly vote for mcp ?? Kodi chisankho ca by-election simunaciwone mene cayendera ? Ku zomba mcp yapezakotu zero then look at kasungu the home of mcp dpp yabwelakotu ndi khansala !!

  52. galu mukamamuyamba alipachean musamaone ngati saluma,muchenjere kuti akangodura pacheani muchotsedwa akatumba samalani a APM mwakhala pang’ono ndondocha zanuzo ziuzeni tatopa ndikutibera misonkho yathu agalu inu

  53. Sanagonje Ibu wanuyo anaba ma vote open your eyes my fellow Malawians some people are not born leaders but you force them to be a leader Ibu has failed malawi is seing a danger warning signs

    1. A Kachingwe mwayankhula zeni zeni. Ati inu Mbuzi, pamene iyeyo ndiye Mbuzi ngakhale Standard 8 sanayione….The most Stupid dpp Kadeti boy! Kusapota zimbaza zi Amalume ake kkkkkkk

    2. koma aMalawi amvekere munya 2019 DDP Boma woteroyo ngakhale K500 ku account yake kulibe kuli zero zero, mind your business ngakhale ku mwalira lero aDPP wo saziwaso kt m’modzi waife no more

    3. Frasher Kachingwe I think were a baby when people voted in 2014 thats why u don’t know who won the elections and don’t allow the politicians to misuse u just work hard to earn a living FULL STOP

  54. Koma mbava za DPP osanama zafika pakuba mwa uchisiru ndikwabwino kusiya kut ena atenge ayendese dzikoli. Ndikunena pano Britain yapereka 193 million pounds yot achepesere umphawi muziko muno koma ayi ndithu akuluakulu athoyolera ndalamazi mmatumba awo kutisiya anthufe tikuvutika.

    Nsanene nkhan ya ndalama zomwe chaponda akubazi linaperereka ndi dziko America kut agule chakudya ku Dziko lino koma Zachisoni ndithu waba ndalamazi . Anthu kut alembe a nkhaniyi mukusekanso pakamwa choona chisaziwike shame Peter Ndi Anzakowo bg up Times news

  55. Anthu ochita zamdziko ndichoncho basi kukanganilana zapadziko cholinga choti alemere nd misonkho yamphawi kma anzelu akulimbirana ufumu wakumwamba ndipo ochita chamuna akuwupeza ufumuwo

  56. DPP ikuthawa chithunzithunzi chake chomwe , 2016 inayenda moyera , yapondereza a Malawi , yapha a Malawi ndi njala , yapha mabizinesi a Malawi. 2017 ino iyembekezere zokhoma bwana weniweni aoneka kuti kuti , kodi ndi iwowo kapena ife timkapita kukawasankha pa mavoti . Chakwera asadane naye chifukwa akulankhula zofuna a Malawi .

  57. Dpp Ali nje nje nje cz of chakwera especially cz they known kuti Ali pampando wokuba from chakwera yemweyo so sangagone naye tulo.dpp mwayaluka

  58. Dpp Ali nje nje nje cz of chakwera especially cz they known kuti Ali pampando wokuba from chakwera yemweyo so sangagone naye tulo.dpp mwayaluka

    1. Anamubela cakwera ? North vote for amayi central vote for mcp & south vote for dpp . Therefore the region with high population z south so hw cakwera who come from minor region b the winner ? If dpp comes from north ur comment would hv make sense

    2. Anabera y mbendera amalira?y amakana kuwerenganso votes and all computer systems hacked thru chilima.u u dont know??? Why akumusemera stoty yoopsa they want ti do treason like they did with casm chilumpha???? Evil pitala and all dpp followers,cashgaters.admarc maize gaters.shame

    3. All those illegularities anganene ndani kuti dpp inawina? Whre in the world munthu amawina ndi 36percent meaning 64persent sinamuvotere.ask pitala will tell you kuti anabera

  59. Mwina kapena ku Malawi mkukhala nawo mbili zolandana boma.But i wil wonder if that happens,MCP has a lust for power since it has been in opposition for 20 yrs now

  60. Bvuto ndilakuti olamula amene alopowa akumuopa chakwela, sizoti azinena zomuyipisa apa n for the way i c its btr one party system timadula makadi ndipo ndalamayo imagwila ntchito zotukula boma than this pipo who are full of corrupted. Pa umoyo nthawi yomwe ndimakula ndinalibe maganizo ozagwila ntchito mayiko akunja koma the way things are it made me left my blvd country. Koma ndimene kwacha ilili panopa olo Mwana wokwawa akuuza zopinda kunja shame on u bingu leave chakwela alone

    1. Ndili ndi history kwambili when it comes to my blvd malawi, that’s i get pissd off when i read what is happening. I was supposed to b back last year already from this underground of mine bt i always get dissatisfied with DPP

    2. Ofunika kwauza ndipo zomwe amati tisiye kulankhula pa social Media pokhuzana ndi president aaaaa chilima what ever u call yrself we are not stupid this where our voice will be heard. Let’s 2lk guys wat we want thru media

    3. Kkkkkkkkkk Kamuzu ndiye akanaletsa Multiparty.kuti isalowe ngati analidi ndi mphamvu.Tsoka mphamvu zinatha ndi Mabishopunso aaaaaaaaa sakanachitira mwina koma kuviomereza.Ngakhale mbali ina amakana komabe zinali zosatheka Malawi waipa basi even akubwera kusogorowo mbava zokha zokha yayipa dziko basi.Ife bola kuno ku SA tikuchita ngatiko ndi Randyi tikatumiza R2,500 ayi ndithu K120,000

    4. Frazer wakamba zanzelu komano ndiangati amene atakwanitse kuti abwele kumayiko amene enanu mukukhalawo, ndalama ya passport yokha panopa ndi plot yonse yamakolo ako kuyigulisa nanga transport kokafikila ndim’bale yemwe alibe life is hard brother. Ingochoka DPP tione zina basi

    5. Analikuti nthawi yonseyi? ndikuona ngati chatsitsa dzaye kt njomvu itchoke nyanga ndi kuba kwa ndalama zomwe a chaponda aba za maize gate. boma liri ndimanyazi kt liyaluka zangoyambika chabe zazikulu zikubwela bingu unatisiyila mamvuto nane ndidzafa kma boma iri lanyanya kuba…

  61. dzikoli ACHAKWELA akuitenga ngt ndikumozambiq et??? zakunyelo basi Ndale zkusokoneza kwambili ndichfkwa chake mwatulusa k2.000 ya solid kupusa basi…

    1. Nyapala inu mukuwona ngati tizakuvoterani Ife aku south ? Majority will rule Malawi forever and we the southerners we r in majority

  62. Yes if u continue to stl our money u wll s in 2019.Chaponda stl alot of money 4us and people nw dying bcz of him.Wat kind of leaders is this?.

Comments are closed.