Ochemerera wa Bullets, Billy One apepesa ku mtundu wa Malawi

Advertisement
Billy One

Modzi mwa ochemelera a timu ya Nyasa Big Bullets, Beleti Severe yemwe amadziwika bwino ndi dzina loti Billy One wapepesa ku mtundu wa a Malawi pomenya mlembi wamkulu mu unduna wa zantchito, zamasewero komaso zomangamanga a Sam Madula.

Billy One anamangidwa lolemba atakuntha  mbama mlembi wa mkulu mu unduna wa zantchito, zamasewero ndi zomangamanga, patangosala phindi zochepa kuti Nyasa Big Bullets ithambitsane ndi Be forward Wanderers mumasewera omwe amalimbirana bus pa Bingu National stadium mu mzinda wa Lilongwe.

Billy One
Billy One (Mu buluku lakuda) ku khoti ku Lilongwe.

Mawu ake Billy One wati iye ndi okhudzika komaso wapempha  mtundu wa a Malawi komaso a Madula kuti amkhululukire pa zomwe anachita lolemba lapitali.

“Ndikupepesa kwa a Malawi onse omwe anamva zomwe zinachitikazi, komaso ndikupepesa kwa a Madula omwe ndinawalakwira komaso banja lawo lonse ndikupempha kuti andikhululukire pa zomwe ndinachita,”Billy one adauza wailesi ina yodziwika bwino.

mmawu ake Billy akuti sakudziwa chomwe chimamuchitikira kuti  afike pomenya  mlembi wa mkulu mu unduna wa zantchito, zamasewero ndi zomangamangayu  kamba koti mutu wake unali utasokonekera ndi utsi okhesa misozi omwe unaponyedwa pa gate pomwe anthu ena amasokoneza.

“Sindikuziwa kuti zinakhala bwanji kuti ndimenye munthu wa mkulu ku unduna wa zamasewero chifukwa pa nthawi yomwe zimachitika izi mutu wanga unali utasokonekera ndi utsi okhesa misozi (tear gas) yemwe anaponyedwa pa gate pomwe anthu ena amasokoneza.

“Ndipo sindimaziwa chilichonse chomwe ndimachita komanso ndinali odabwa nditazindikira kuti ndinamenya mlembi wa mkulu mu unduna wa zamasewero chifukwa pa nthawi yomwe zimachitika izi sindimayakhulana ndi mlembiyu ndikupepesa kamba ka zomwe ndinachita,” adaonjezera Billy One.

Billy one yemwe ali pa bail pakadali pano azakaonekeraso ku bwalo la milandu pa 21 January 2017 pomwe akakhale akupitiliza kuyakha mlandu ovulaza munthu.

Advertisement

140 Comments

  1. Indeed kupepesa uku nkwaboza wabullets sazatheka they dont av manners they are 100% ignorant thats y they called themselves palestines they aren^t malawians mmalawi amakhala wa ntendere dont trust bullets fans

  2. Billy one knows why he had to hit him. That’s not the correct reason. He’s just saying that coz the so called victim has some powers next time don’t slap him use a gun if possible

  3. Tiyeni tiwakhululukile masapota onse abulesi komanso tiziwaikiza m ‘mapemphelo kuti auziwe mpila, chifukwa mpila sinkhondo, mmmmmm ndikumva kukoma 5 -1 mbava inu ambuye akukhululukileni
    :

  4. Makolo ako sanakulere bwino ntchifukwa chake khalidwe laki ndilonyasa.Ask everywhere civilized people never fight kima izi dzikuonetsa kuti kunthundu kwanu ndinu achoncho.Sinthani abale chaka cha tsopano ichi

  5. Chabwino ife aBullets mbuli,zigawenga inu ophuzila Arobert muli ndi phd mumamwa mowa wa bwino eni cash gate dziko ndilanu ili osamakankhula mokhadzula

  6. Timu imeneyi izisewera kumatimu ang’ono ang’ono basi chifukwa nthawi zambiri amayambisa ziwawa anthu ake ndi amene .Abbilly akhale zaka ziwiri osawonera mpira uliwonse mdziko muno

  7. Ukayambe wabwezera ma mirror glasses and ma Toilet omwe waphwanya ku Bingu International Stadium, then Uzipepesa bwino, Otherwise go to hello with your sorry ,thief criminal

  8. Zoona zake ndizoti a Bullets ndiomwe amasokoneza masewera ampira kumalawi.Chitsanzo anali kuLilongwe posachedwapa stadium ya Bingu kumeneko kwabedwa zinthu kuti tifufuze ndiomwewa a Bulletswa.

  9. Ngat Muthu Wapanga Zaugalu Mubwezeleni Zake Zomwezo Koma Ngati Sanalakwe Musamupange Chilichose. Ndie Enanu Musapezelepo Mwayi Onena Mzanu Kms Ngat Adamumenya Zilibwono Chifukwa Amudziwitsa Line Tiyenazoni Anyasa

  10. Ambiri mumatenga mpira kukhala mulungu wanu ndie chomwe chalamula ntima wanu mumachita chomwecho. Sory kwanonse amene mumalephera kugona kupemphera chifukwa cha mpira. Mulungu azaona nanu chochita tsikulina

  11. Very absurd, disgusting, pathetic, uncalled for, embarrassing, unruly, barbaric, talibanic, boccohallamic sort of behaviour. shame on you Dude and all your fellow nyasibibi diehards. I rest my case.

  12. Imeneyo Ndiye Bullets Kwawo Ndi Kuba Kupha ndi Kuononga Anthu Osavomereza Ndi Otani? Amenewa Kodi Mukafufuza Si Ana Agulu La Boko Halamu?Ana Anjoka!

  13. Anthu aphuma ngati achina Billy azipasidwa ka chikoti kenakake kti ena azitengelapo phunziro,,sizopepesanzo ai,azipepesa akulira

  14. Ife Zikutikhuza Bwanji? Iyeyo Anamenya Ifeyo Ngati? Apepese Mzake Amamenyana Nayeyo, Musatisokosepo Apa Ndi Anthu Osaziwika! Pano Tilindizochita Tikudikira Admarc N Cash Gate Cases!

  15. Billy one don’t say u didn’t know what u were doing bcz this is ur habit. U were arrested b4 bcz of the same conduct, but now u know kuti munthu unampanga chipongweyu ndi olemekezeka. Ur excuse about tear gas is not valid bcz it’s not only u who got affected bcz of that tear gas. Iwe ndi munthu m’modzi mu gulu la anthu osokoneza masewero a mpira wa miendo Ku Malawi. And I Wonder why u r called flames chief supporter bcz according to my opinion u don’t deserve that name. Such an abuser like you

  16. OCHEMELERA BULLETS AMAONJEZA ATENGELEPO PHUNZIRO NDI OMWEWOSO ANAONONGA KATUNDU KOMA ADZIWE KUTI AMAONONGA CHITHUNZI-THUNZI CHA TEAM YAWO YA BWINO IJA

  17. Musanene kuti waonga mbili ya Bullets kulibe komwe wa Bullets adakhalapo ndi mtendere awine aluze chimodzi modzi siyekhayo Vuto ndi team yomwe inadzadza ndi zigawenga mbuli osowa zochita .inu musayankhule ngati anzeru Bullets imadziwika ndi uchifwamba zoona zake

    1. Kkkkk a bullets tangokhalani pansi musatibowepo apa…..amuna anzanu ali Ku pelete uko ndi mi mfuti pita ukapange mfwe mfwe ngati siukadyako jombo kkk

    2. Kkkkk a bullets tangokhalani pansi musatibowepo apa…..amuna anzanu ali Ku pelete uko ndi mi mfuti pita ukapange mfwe mfwe ngati siukadyako jombo kkk

    3. Palibenso zotiwina atiwopsyezeapa chomwe timaziwa malawiyonse bullets sichimatha chaka osanva amaba ndalama pa Gate, agenda magalimoto anuwake, amathila mikozo maplayer a team ina, iiii amamenya azimayi amalonda, zikatele iiii player wakuti wamenyedwa kkkkk team ya mpila imeneyo? Chomwe ndimaziwaine oyitanila ma Tex ndi ogulisa katundu osapachika palumali amakhala opanda nkhalidwe

    4. Mwayiwala anakupatsani chilango chosamenyaso mpira pa Kamuzu stadium chifukwa chopanda khalidwe a KAPADO INU..mapeto ake anakupatsani pa Balaka kupha konso munthuso okhala sapota wanu agalu inu

    5. Man ndinu opusa mwanva inu school yake iti yoti ndikunyozera azanu kuti mbuli iwe bwera tionetsane ma paper tione dolo kape or ndalama ulibe WHAT THE FUCK. Usamayese uzayesapamamwa umaphatikize galu iwe, ukunena ife mbulu pomwe makolo ako or a sadziwa komwe komwe anayang’ana

  18. ngati wapepesa mkhululukileni poti samkadziwa chomwe amachita koma chisakhale chizolowezi.

  19. Kdi Enanu Mumangoti Umbuli Ku Bullets Ndye Kti Ku Club Yanuyo Kulibe Mbuli ? Kuli Anthu Ozindikira Okha Okha ? Kupusa Basi Iweyo Ndiweso Modzi Wa Mbulizo Ku Club Yako

    1. Hahahahaha Waziiwala Iweyo Kti Ndwenso Mbuli Yaikulu , Umbuli Wako Waupanila Wayamba Kuseka Wanzako ? Hahahahahahahaha

  20. Kdi Enanu Mumangoti Umbuli Ku Bullets Ndye Kti Ku Club Yanuyo Kulibe Mbuli ? Kuli Anthu Ozindikira Okha Okha ? Kupusa Basi Iweyo Ndiweso Modzi Wa Mbulizo Ku Club Yako

Comments are closed.