A mad man managed to make his way into the Kamuzu Palace in Lilongwe even though the house has several checkpoints, Malawi24 can report.
According to reports, the mentally ill man was found sleeping in a waiting room within the palace before officers on duty managed to detain him.
The man has since been taken to Kawale police for questioning but is expected to be sent to Zomba mental hospital soon.
The incident follows another one involving a large python that was found at the Kamuzu Palace over some months ago.
During late Bingu wa Mutharika’s era, the palace was reported to have been stormed by ghosts.
Sponsored
197 thoughts on “Man breaks into Malawi State House”
Comments are closed.

Amafuna kukacheza ndi wamisala mzake
Anthu inu simukuziwa chilichonse ndi Ana inu peter ndi wakulu sangakhale alibe kenakake inu state house wamisala alibe mpata olowa iye ndi zomwe peter amasunga nyumba mmo ndiye watha mphamvu zake zomwe amasungila bola kuthaya akhale ngati wamisala ukafunsa monva kuti ndi mulomwe wa kuThyolo pa 6 miles
Kkkkkkkkk kodi state jouse ndiyimeneyo mmmmm bola ndata
Kikikikikiki aaaaaa palibe vuto poti ndi wamisala basi saziwa komwe akupita
Mmm ndondocha za a pulesident
only to warn ceaser to be aware of ardes of match
Kkkkkkkkk
koma abale nkhanu yolemba inasowa eti
kkkkkkk achitetezo aku malawi
Its a new year for sure guards were’ sleeping after heavy drinking.
Malawi24 yayamba boza amasowa cholemba ndianthu opusa amenewa kodi ndindani amawauza kuti azilemba nkhani zonama pa fb
Kikikikikikikikikikiikkikikikik chitetezooooiikoma bomaloli ndi chipsyinjo chaA the ndithu aaaaaaa
So who cares
Amakapereka uthenga wa njala ameneyo kwa big man.
That’s impossible unless he is one of the guards or wina mwamupengesa from inside
Spirit of death ija amati muwapemphelere ndiyimeneyo kkkk
Pay back time