Lightning kills couple

Advertisement

A couple has died after being struck by lightning in Mangochi district.

Mangochi Police Deputy Public Relations Officer Amina Daudi has identified the two as Yusuf Mbalako, 66, and his wife Annie Akibu, 56, both from Chilinda village, Traditional Authority Makanjira in Mangochi.

Daudi told Malawi24 that the two went to their garden which is few meters away from their house and whilst there rainfall started.

They decided to return home but suddenly a lightning struck them on the way and were pronounced dead at Makanjira Health Centre.

Postmortem conducted at Makanjira Health Centre revealed that they died due to lightning shock.

Advertisement

60 Comments

  1. Pulani yomwe mwaipanga Ku malawiko sopano ndi imeneyi yophela anthu ndi imeneyi ?ambuye lowelelaponi woipayi asakhale ndigao zolinga zake zisakwanilitsidwe

  2. Muzonse tiyamike Mlengi ngati kulikufuna kwake. koma ngati Iyiso! Ili plan ya woipayo, Takweza maso kwa inuso! Mlengi mulowelelepo mutiteteze ngakhale timakuchimwilani komabe ndi ife Ana anu. kupanda kutero tintha ndithu!.

  3. God is not killing anybody, but He is allowing it to happen, kuti anthu tidziwe kuti tili masiku omaliza. Before anything happens, Mulungu amakhala atadziwa kale, and He has all the powers to not let anything happen. Koma akulora kuti zichitike so that we cn b alert. Thts wat I meant.YAMIKAN

    1. Pali mau oti khalani maso nthawi ina iliyose,, chifukwa imfa imabwera ngati wakuba,,,, tikhale okonzeka m’mitima yathu,,,, Mulungu akudziwa tsiku ndi imfa ya tonse pa dziko la pansi pano,,,, tonse sitingapite kumwamba kudzera nkudwala ayi!!!!chachikulu tidzikhala okonzeka. Every time!!

Comments are closed.