BREAKING: Ndau fired as Information MInister, Dausi replaces him

Advertisement
Nicholas Dausi
nicolas-dausi
Dausi: Back at Information Ministry.

President Peter Mutharika has axed Information Minister Malison Ndau and replaced him with vocal ex lawmaker Nicholas Dausi, Malawi24 can confirm.

This has been confirmed in the seen chief Secretary to the Government George Mkondiwa being replaced by Lloyd Muhara.

Mkondiwa has since been redeployed India as High commissioner. He replaces Dr. Issac Munlo who will now be Chief Director in the Ministry of Foreign Affairs and International Corporation.

Mutharika has made several changes to his cabinet atleast three times this year alone.

WE HAVE MORE REACTIONS TO COME.

Advertisement

131 Comments

  1. kkkk dziko lino linadzaza ndi anthu amamina mmutu okhaokha sitingatukuke,,,,they keep on recycling old fashioned people to hold ministerial positions,,,period

  2. Zadziko Mzosiirana Andau Mungopita Ku Mcp. Nao Adaus Adatopesa Nthai Ya D R Banda , Muluz, Bingu , J B Lero Kwa Pitala Ooooooooooo Ngat Kulibe Wena2

  3. “May ur xmas be free from quagmire …. let it be adoriferous, full of rampant cockistocracy, aggravated by the vitality of perambolity with the plumage of decapitation so that the new year will be congruental in as far as the mototiplity is concerned” Dausi happy festival quote

  4. Mr Ndau,life goes on don’t worry. Mr president, for taking in Dausi, Ihave seen you doing agood job for the 1st time. Mr Dausi welcome.

  5. wlcome MR DAUS its long time we here u r voice , koma atola nkhan mulimbetu ndi chingelez ch an nkuluyu muzinva koma ?apa ndiye oxford dictonary izi khala pafupi chonde

  6. kaya ndi Dausi or Ndau ine palibe chomwe chisithe m’moyo mwanga but ku ma family kwa awiriwo aona kusintha or muzamuike Aunt Tiwo pa mphando umenewo changabe palibe

  7. Nanunso Amalawi 24 Mwanamapo Kanu Kachizungu Kosatira Dausi Ati(president Peter Mutharika Has Axed Infomation Minister) Kkkkkkkkkkk. Apatu Zikuonetsa Kunama Kwanu Zoona Apresident Angatenge Nkhwangwa Ndikukhapa Nduna Yawo?Ayambana Chani?Kkkkkkkkk Dausi Tiyenawo Aphunzitse Amalawi 24.

  8. eeeya wakumana nazo, APM amadana ndi mabodza, mesa unkanamiza dziko kuti alibwino pamene anafa ziwalo ali ku USA, wauponda

  9. Koma a dausi uku kukhoza kumaliza kwao chifukwa zinthu zafika povuta chilungamo sungalimbane nacho ndiye poti adausi amalimbana ndichilungamo ndiye ntchito yawo chabwino

  10. Mr Ndau is a victim of access to information bill (ATI). He will be rememberd as the minister who brought the ATI bill in parliament despite his party not willing to pass it. The other thing mr Ndau being a reverend was suitable for this job of information minister. This post requires someone who is naturally a lier not some reverends who believe lying is sin.

  11. Acording to my apabango he is good dausi,kkk ma dictionary manja guyz,akwarkwangu wafika,we have more reactions to come,dalayu amapangitsa dpp kumvetsa sugar.Ndi adala pa ndale,ndamufira.Kkk no quarry here kkkkk dausi mwini oxford,not pakachere dictionary imene ndau ama user.Kkk zilikuno

  12. I am actually phlegmatic over this scandalous news..just yesterday they were jubilating during the awards now you’re hacking him off the office??…this is hellish and helibent,helical cracking,..not this hedgehog…!! kkkk

  13. ehe nde mwat Dausi? dikirani muone ndale zikome. Ndikale lija zinakoma . kkkkkkk M’dala amakometsa ndale uyu… Am not saying am happy with the firing of Ndau but I missed this vocal politician so much!

    1. sindinapite patali ndixul koma secondary level tinathana naye.my english teacher,said to me:simple english is gud english.ngati ena sakumva zomwe ukuyankhula ndekuti ndiwe mbuli.Dausi saziwa chizungu koma grik.

    2. Though i av neva went to college/university,Dausi samaziwa english,i observed tht on questions&answers with mr dausi,mayb we must say he’s fluent in english

  14. No wonder is fired from cabinet, not because of poor performance but has no root’s in DPP and he is a Reverend by professional and DPP believe in Lie’s not in love

    1. Ndau ndindani? ha ha ha ha ha!! Tamufuseni ndauyo kuti kudela kwanthu wapanga chani ndichulungamo chakecho chiloweleni boma mmmm 0 pa 10 ndipo eee amuchita bwino akungodya ndalama osapanga chitukuko amene akuti osadziwa kunamayo

Comments are closed.