Man impregnates teenage daughter

Advertisement
Rape

Police in Kasungu district are keeping in custody 35- year-old man for sexually abusing and impregnating his own 17 year-old daughter.

Public Relations for the Police Station Edna Mzingwitsa said the rapist who cannot be identified separated with his wife last year and the woman together with the girl left the couple’s home.

Rape“But in January the man went to the wife’s home village where he took the victim to be staying with him,” she explained.

However, when the two were staying together the father began raping the teenage girl and eventually she got pregnant.

After discovering that the father is responsible for the girl’s pregnancy, the wife of the suspect reported the matter to police.

The evil father has since been charged with incest in accordance with section 157 of the penal code and will appear before court soon.

Advertisement

66 Comments

  1. Azibambo wena kupanda manyaz kutulutsira mchira mwana obereka okha.heee!! Thats shame 2 that idiot man.if it were my father i wud chase him away.

  2. koma Guyz sindiziwa ngati mumasatira bwino tsambalino,koma azanthu Achigawo cha Kumpoto wa! pakhani ngati izii! Akusogora why?. sizotindikunyoza koma pakafukufuku wa nkhani zogwirira kuphana cz za akazi zikuchulukira kuchigawo chimenechi! tapangani kafukufuku panokha mundisimikizira izi.

  3. Khuku ikuyenera kumwa madzira ake so he’s not first person even Roti mkaazi wake atasanduka chulu cha nchere adachinda aana ake

    This thing zidayambika kalekaaaale

    1. Dont offend the bible ….Lot wanted to protect visitors from the merciless and offered his dotas by the grace of God it did not happen and not him (LOT).

  4. Vuto la ku thamangiranso ku kwatira ndi limeneli! Kutereko mwanayo ndiye kuti anamubeleka ali ndi zaka 19 kkkkkk! Ndiye kuti kukwatira anakwatira ali ndi zaka 16! Mmmmmh shame! Chonchi ziko silingatukuke tizingonyenga ana obala tokha basi

  5. Vuto la ku thamangiranso ku kwatira ndi limeneli! Kutereko mwanayo ndiye kuti anamubeleka ali ndi zaka 19 kkkkkk! Ndiye kuti kukwatira anakwatira ali ndi zaka 16! Mmmmmh shame! Chonchi ziko silingatukuke tizingonyenga ana obala tokha basi

  6. Koma kaya ndivizimba koma zoona munthu ukakwate mwana wako ndiye momwe chimakomera chigololo ukamadzera ndiye mpaka mumatchulaso baby apa wandimaliza mwanayo asaaa

  7. Kod Anthu Ngat Amenewa Akuculukira Culukira Bwanj? Pakufunika Cilango Cokhwima Kt Mwina Athawa MKumaopako.Koma Ngat Simutelo Inu Amene Mmatiimilira Ngat Bomanu Nngakhale Kuti Mumapanga Ciganizo Mocedwa (very Very Slow) nde Eeee Ana Akaziwa Tingoyamba Kuombera Cifukwa Zikumatisokonezera Dziko Ndso Population While Tili Paumphawi.

  8. Muzinena maina awo awo osamawabisa tiziwadziwa…just incase tikamakaona azibale mundendemu tizikamva maina mawo and to see how stupid and merciless they look personally..

  9. Ndiye kuti anawa akukoma kuposa,amawo, every week mwana akudyedwa ndi bambo ake…boma lathu likanafufuza chimene chikuyambisa b4 its too late unlike kumangowamanga anthuwa…

    1. Ukamat Achewa Umafuna Kumalimbananao Mesa Nunthuyu Ndmtundu Wako Nde Ngat Ufuna Ukambidwe Ungonenena Titha Kukusata &uleke Kumakamba za Achewa, Zotisokonezele Cikhalidwe Cathu Sitimafuna

  10. Malawi walero… Abambo kudya zoti ankachotsa bibi okha lero chifukwa wayamba kuzikhula yekha abambo mbongeza kufufuma ngat jeke otukulira truck

Comments are closed.