Wanderers fan banned for a year

Advertisement

A Be Forward Wanderers fan has been banned for a year having slapped a referee who officiated the team’s match against Civo United on 15th October 2016, Malawi24 has learnt.

The fan, Charles Lizigeni had slapped the referee after a few decision the ref made.

According to the Super League of Malawi (Sulom), the conduct displayed by Lizigeni was un-called for and not condoned.

”We would like to commend the quick action shown by the stewards and police on duty who managed to apprehend the culprit” a statement signed by Sulom’s General Secretary Williams Banda reads in part.

Advertisement

26 Comments

  1. Kumeko ndiye kukhara.Apa chilungamo chayenda ngt madzi.Ine ngt m’modzi mwa wanthu okonda nyerere ndawombera kuphazi kamba kachirangochi.Musayiware mayi anga anandiuza kt ndisasapoteso timu yina koma NOMAAAA!!!!!Akundiuza sananenepo kt tizimenya othandizira oyimbira.Zochitsa manyazi Zachitikazi.Ndikupepesa m’maro mwa anthu ose amene timayinyadira timuyi.

  2. Si inu mumati team yanu ndi ya anthu ozindikila nanga izi ndiye zitiiii osamatha mau kwanukonso kuli osasambaaaaa nkhalamba ngati uyu onyeledwa uja mumati vale mizele kkkkkkkkk

  3. Anthu tonse amene tikuziwako kumene kuli ma ofesi a News 24 tipange tsiku tipite komko akawaxidwe makofi ngati akumasowa zolemba ulibwino kumapita kumakapalira chimanga ndikutsiyana mkumalemba nkhani zopanda mitu apa. Apa sipodanitsa anthu mwava zoputsa basi.

  4. Who will be having an eye on him that He doesn’t patronize football matches? Is he a famous person that people can easily identify him?

Comments are closed.