Mayi amangidwa kamba kogwilira bambo

Advertisement
Sex

Apolisi mu boma la Machinga ananjata mayi wina wa zaka makumi awiri ndi mphambu zisanu ndi imodzi (26) ati kamba kogwlira bambo wina wa zaka makumi awiri ndi mphambu zitatu (22).

Malinga ndi mneneri wa a Polisi mu boma la Machinga, mu mwezi wa Okotobala chaka chomwe chino, Mayi Inness Salamba ati anagwililira bamboyu.

SexIwo anati Mayi Salamba anaitanila bamboyu kunyumba kwawo, ndipo atafika kumeneko iwo anavula ndi kumukakamiza kuti agone naye.

Ati bamboyu atapita kwawo anaoneka otopa ndi osokonezeka ndipo atafunsidwa, iye anaulula kuti wachitidwa chipongwe ndi mayiyu.

Apa akuti achibale a bamboyu anakaitula nkhani kwa amfumu amene ananena kuti nkhaniyi apite nayo ku Polisi.

Atamva zoti nkhani yakatulidwa ku Polisi, ati Mayi Salamba anathawa osaonekanso.

Iwo anaonekanso mwezi uno poganiza kuti nkhani ija yaola, koma anangofikila mmanja mwa a Polisi.

Iwo atengeledwa ku bwalo la milandu posachedwapa kukayankha mlandu ogwililira ndipo akapezeka olakwa atha kukakhala kundende kwa zaka zisanu ndi ziwiri (7).

Advertisement

220 Comments

  1. Ayawo ndi ambere chire ma man polo ndi first priority yawo angagwiririredi kkkkkkkkkllkkl

  2. don’t talk nonsense.just remember rape ndikugonana ndimu2 mokakamiza asakufuna nomater anampangisa kuti axuke

  3. Kkkkkkkkkkkkkkkkk ine nde zangondsekesa kod zmayiyo alibe amuna ake kapena alinawo azmayi ena kuchitisa manyaz ok bola dolo waufila bas ndili ine sizngatheke guys kkkkkk kma kumalawi hey kwafikapo

  4. ine chiti ndikambe ndichi ano ndi masiku otsiliza amuna omwe sanamudziwe yesu maso auzimu adzawasowa kuti azindikile oipayo ali pafupi uyutu nde oipayo satana wafika pamenepa zovuta

  5. palibe ngati wagwililidwa akasume basi kkkkkkkk mwina wagayila matenda komasotu guyz pali akazi ena azimphamvu osamangotokota apa kkkkkk komaso ndani amene angalimbe atagwilidwa shaft ndi mkazi kugwililidwa it does not mean all u are saying it is doing it unwillingly ngakhale analowesa yekha after kumugwilagwila iye asakufuna anagwilila basi don’t take it too funny this is bad

  6. Kodi abale ndi chichewa chathu chathu cheni chenichi chizitivuta kulemba zoona? Makumi awiri ndi mphambu zitatu(22)????! Muziyamba mwawelenga kaye nokha pilizi.

  7. Fuso lina mkumati kodi ali adimited ku hospital…kkkkkk aaaaaa zina ukaona kamba anga mwala…mmasule mzimaiyo wamulakwila ndiithu. Mmene zimakomela muja? km galu ameneyu..hehehehehe!!!.:…

  8. Kkkkkkkkkkkkk nkhani zake iii sichina amuna mwanyanya kuchona ku south africa ndemwati mkazi akatopa angapange bwanji? Mkaziyo siwolakwa asamumange

  9. Nkhani zina…..mtheradi umaona ngat ukulota ukazibva.Moti ndi nkhani yonena ku police imeneyi.Iye amabva akupanga zosapanganazo?

  10. Aaaaaa xacamba et angomunanizr mzimaio pakat pa mamuna nd mkazi angamugwirire mzake ndndan ngat anatota sanamugwirire koma ngat sanatote anamungwirra. Guyz zingatheke kugonana nd mkaz usana tote? Kufoira et kkkkk.

  11. Koma nkhani iyi yandiseketsa kkkkkkk nde mwati nkaziyu ali ndi mphavu zotani zompanga force mamuna kkkk nde mpaka nkuluyu anawutaya kkkkk ine zandisangalatsa ndagwa ndiphwete

  12. Ndi bambo otani ameneyu? Akuti anakafika kunyumba ali otopa kwambiri? Kutopako ndiye kuti wapatsidwa mimba ameneyu. Ndiye ngatidi bamboyu watenga mimba amusamale ndani poti mayi ogwirirayo mwammanga?

  13. koma man munachita bwino kupanga report ku police ayenela amangidwe ameneyo osangoyendera poti nkazi apezeka ndinyenge ayi guys kunja kuno kuli matenda amulakwira nyamatayo mwina ali ndi nkazi amene anagwirizana zochita si bwino akamupatse matenda nkazi wake wosalakwa she derceve 8 years in prison for rape case

  14. Bambo chitsilu chakanthu, mayi tsagwirira anayifuna kungoti bambo kubed tsakudziwa . Anthuni mudzitumidza nkhani dzachikoka otsati zolephela kubed ngati izi , bambowe mpaka kukanena Ku police bwera ndizakulipire mlandu mayi anavutika ndiye otsaziwa kuti unagwa mupapa .

  15. Kunena zona pakufunika kuti maiyu alandile chilango chokwana chifukwa ndikulakwa kukupangira chinthu chimene iwe mwini sunafune ndichimozimozi amuna ngati angwirira mkazi yemwe sali wasaizi yako amati wamuphwanyira ufulu wachibadwidwe nanga mwamunayu sanaphwanyidwe ufulu wachibadwidwe ?? MWINA Ali ndimatenda ndiye kuti amupatsira amuonongera tsogolo lake

  16. Apa chakula ndichibwana…. mukadzakumana nazo mpamene mudzadziwe kuti kodi mzothekadi mkazi kugwirira mwamuna? Koma choti mudziwe ndichoti azibambo ndi achinyamata ambiri awumirizidwapo (kugwiriridwa) ndi azimayi. Kungoti timawona chinthu chamanyazi kuti tibwere poyera .

  17. Pali zina zot ukanva ansala kumaiona wekha.fuso anali pambwamba panzake nndani nanga abamboo anamangililaa kodi pokanika kuchoka waboza kkkkk

  18. Paja kuti adagwililira iye mamuna sanakhojele koma sanatote paja adotowo adamuyesa kuti zose sanachite mayi amagidwe paja mamuna adachinda kadziyo amutayi

  19. Ndiye kuti naye mwamunayo amafuna,kunena mosapsatira anadzuka bwanji,?or kuti misempha yagwira ntchito yake nde basi kungoti njoo! agwilirana amenewo asaname

  20. Koma nyamatayo ndi kape ,that is not Rape ,nyamata (22) years wa mphavu zake angagwiriridwe nd mayi wa zaka 26 ,that is a lie ,investigate wisely

  21. Azimay ena amatero kaamba kofuna kumupatsa zizobodola mamunayo atsagane naye kumanda shit…osayifunafuna galu ikutombe bwaa..mumve kuwawa

    1. mamuna sangagwililidwe ndimkazi coz mbolo sitota ngat sukufuna choncho siingaloweso ku nyini. amazifunaso adawo

  22. achimwene ogwililidwa,nali funso: zinatheka kutelo bwanji musakufuna?munachitapo chani mayiyu atangoyamba kuchita zodabwitsa? musatinamize mumkafunana ndikale ndiye mwangosintha maganizo,ndikovuta mlanduwu inu kuwina oweluza ngati ndi achilungamo.Mukungozumzitsatu apa mkazi wanuyi malo moti mutiuze kuti mwapeza.Mukanangomangitsa chinkhoswe nkuyambapo banja mmalo moipitsa mbili ya wachikondi wanuyi,sanakugwilileni koma kuti mmakondana bwanji simunathawe kapena kukuwa? bodza silabwino musapweteketse munthu wosalakwa,awa ndi akazi anu chonde akondeni ndipo maso awo anayamba mwano,amuna ena sayesa kanthu koma inu nokha basi ndiye inu mpaka kuamangitsa adona amatelo? pitani mukasekese mlandu ndipo apolisi mukauze kuti nkhani yatha chifukwa ndi mkazi wanu.

  23. Mayi amangidwa kamba kogwilira bambo By Mwayi Mkandawire November 17, 2016 New Military Flashlight Every Patriot Needs to Know About ? Apolisi mu boma la Machinga ananjata mayi wina wa zaka makumi awiri ndi mphambu zisanu ndi imodzi (26) ati kamba kogwlira bambo wina wa zaka makumi awiri ndi mphambu zitatu (22).Malinga ndi mneneri wa a Polisi mu boma la Machinga, mu mwezi wa Okotobala chaka chomwe chino, Mayi Inness Salamba ati anagwililira bamboyu.Iwo anati Mayi Salamba anaitanila bamboyu kunyumba kwawo, ndipo atafika kumeneko iwo anavula ndi kumukakamiza kuti agone naye. Ati bamboyu atapita kwawo anaoneka otopa ndi osokonezeka ndipo atafunsidwa, iye anaulula kuti wachitidwa chipongwe ndi mayiyu.Apa akuti achibale a bamboyu anakaitula nkhani kwa amfumu amene ananena kuti nkhaniyi apite nayo ku Polisi.Atamva zoti nkhani yakatulidwa ku Polisi, ati Mayi Salamba anathawa osaonekanso.Iwo anaonekanso mwezi uno poganiza kuti nkhani ija yaola, koma anangofikila mmanja mwa a Polisi.Iwo atengeledwa ku bwalo la milandu posachedwapa kukayankha mlandu ogwililira ndipo akapezeka olakwa atha kukakhala kundende kwa zaka zisanu ndi ziwiri (7).

  24. Pafika zinthupa ngati ukuchedwa kumufunsila uyembekezere kuti akufunsila iyeyo akadzi atopa mbwiyache ndiye iwe kumangonyada nayo ndodo yakoyo azikuchindani choncho sanalakwise mkaziyo anatotopa naye ndi munthu mauka amamuyabwa ,koma tamufunseni mzathu ogwililidwayo kuti sanamve nawo kukoma?

    1. Kkkkkk koma guys ndye mmene zimakomela muja, mpaka ukasuma kuti wandigwililila kkkkkk zamanyazi….its tru kuti sanaike yekha mwamunayo panbowopo…kkkkkk bola apa guyz

  25. Kodi iwe unagwa mumtengo wapapaya, mpaka kulira kuti akugwirira. Panti wang’ambikayo ndi uti, tandionetse ndithu kulimba mtima kukalowa ku court ndi mulandu umenewu kuteroku mnzimai wamangidwa kuti amakugwiririra? Iwe munthu sukulu unathawa kale, si iwenso mwana pamenepo ulindi udindo kale wapakhomo pako. Ameneyo ndiye, anakati azikupatsa yeni-yeni yapansi panyanja.

  26. Palibepo mlandu apa komanso iwe admn makumi awiri ndi mphambu zitatu zingakhale 22 ??? Mwinatu chifukwa kwabwera two thousand imodzi ndiye masamu akuvuta eti?

  27. Sanamgwirile anarchist kumangililidwa 22years amatani kuthawa or kumukankha ,,,, Anafuna nayenso muziti amapanga chiwerewere osat amagwirirana no!!!!!!!!!!!!

  28. Anagwirizana mbolo ilowa bwanji yosatota?mmasuleni mzimayiyo mesa kufookako ndye kuti anathyapula ma round awiri ndye kuti amava kukoma.

  29. RAPE (Sec 132 of Penal Code). Capacity To Commit Rate. Any person is capable of committing RAPE…Except: 1. A woman 2. A boy under the age of twelve years. 3. Husband and wife, unless it is proven that they have been separated by the court and that they are living apart. Dzivele mtolo mkazi samagwilirira…!

  30. Kodi mbolo imatota ngati mwini wake sufuna? Ngati mayi wagwililira imalowa bwanji ili yofota? Musatinamize apa! Anthuwa amachindana mwa program.

    1. Kkkkk zamatenda uko….coz nkhani ndiyonyengana apa. Zatheka bwanji ma round atatu iliyofota shaaa sindikunvetsa ataa… Good news ngati iyii…mkumati wandigwililila koma bongwe bs..

    1. Zonyozana ayii apa. Aliyese amagwidwa nyere. Nkhani ndiyoti mwamuna salowetsa asatote. Mmai wabwino ngati, en zaonetselatu kuti panalibeso zolipilana…kkkkkk km amuna enawa kumbwambwana man…yhoo!…

  31. Za ziiii, ndiye tiziti chiani pamenepa, mkazi wa zaka 26 sangagone ndi mwamuna wa zaka 23? Ndi woofoka ameeyo bamboyo akanamwa khuzumule uja timati viagra kapena Sildenafil citrate mkazi ameneyo akanachonganso koma mpaka kufika kwao wotopa ndi wofooka zomwezi?
    Mkazi ikamgwira nyere kodi mungamuthe. Nthawi yonseyi wosakuwa nkumakanena kwao apo mwinanso anakauza ami ake za ziiii.
    Zongoopsera matenda omwewa koma ngati kuli kwathganzi wadya zake m’bambo ameneyu kkkkkk

  32. Za ziiii, ndiye tiziti chiani pamenepa, mkazi wa zaka 26 sangagone ndi mwamuna wa zaka zitatu? Ndi woofoka ameeyo bamboyo akanamwa khuzumule uja timati viagra kapena Sildenafil citrate mkazi ameneyo akanachonganso koma mpaka kufika kwao wotopa ndi wofooka zomwezi?
    Mkazi ikamgwira nyere kodi mungamuthe. Nthawi yonseyi wosakuwa nkumakanena kwao apo mwinanso anakauza ami ake za ziiii.
    Zongoopsera matenda omwewa koma ngati kuli kwathganzi wadya zake m’bambo ameneyu kkkkkk

Comments are closed.