Breaking: DPP’s General Secretary Eckleni Kudontoni dead

Advertisement
kudontoni-eckleni

Ruling Democratic Progressive Party (DPP) General Secretary Eckleni Kudontoni has died in a terrible road accident this morning, Malawi24 can report.

According to reports, he died after his Toyota Fortuner’s tyres developed a fault causing the vehicle to roll over several times.

kudontoni-eckleni
Kudontoni: No more.

It is said the accident happened at Bua in Kasungu. He was traveling from Kasungu to Karonga.

Sources say he died on the spot.

As this report was posted, the DPP was yet to make a statement on the matter.

MORE TO COME.

 

Advertisement

219 Comments

  1. Koma guys tiyeni tizikhala ndichisoni atakhala abambo kapena nchimwene wako ungave bwanji umasamala poyakhula kuno ndikunja kumayanja lichero

  2. A Malawi tiyeni tiziopa Mulungu muchowonadi osati kumangokamba pa kamwa ayi,,,, tisanyoze mtembo coz ifenso mmawa ndi mtembo ,, dziko la malawi anthu ake sitimakondana thats why tikumaphana pofuna kt tizidyelera bwino za dziko lapansi ,,, koma zonse tikupangazi Mulungu akatiponya ku moto coz kwa Mulungu kulibe lawyer,, kuli kuimika kt chilungamo chisaoneke ayi,,,

  3. Umoyo wamunthu umakutilidwa ndi zinthu ziwiri: ubwino ndi kuipa. Omwe amaona ubwino pa munthuyu ndi omwe akukhetsa misonzi pomwe amene amaona kuipa kwa munthuyu ndi omwe akunena za kukhosi kwao. Posatengera ubwino kapena kuipa may i say RIP!

  4. Ndilibe problem kaya wina azifa kaya adwale mkono ine ndilibe PULOBULEMU. KKKKK

  5. maike G jinard inuo mutu mwanu mwazaza mamina ndipo mulibe umuthu mwava maliro ndi maliro zopusa mwalembazi musazalembeso iwe ndie ndani kutuwa sanachite kufuna olo iweo lero ukhoza kufa mulungu atafuna ukumva guys mukamalata zopusa ine zimandikwana naliro omwewa paka mwapeza khani ana agalu.

  6. Very good example inu a DPP Mumaiwala kuti muzafa,kulalata,kuba ndi kupha mulibe nzanu bola ngati munakumbuka sacrament la kulapa

  7. There z no way a normal human being can rejoice over another somebody’s death. Ask urself kuti where wil u end. I dont think kuti Mulungu angakondwe nazo zimezi. Ili ndidziko. R I P. Sec

  8. Nde mwati o Ekelesi Kidontoni onakwe bulu ulendu wokatembelera onthu o Mulungu o Chakwera? Ha, zoona bulu kumkwapula kuti omange kowasi osadziwa kuti pa Buwa paima mnjero ndi lipanga lokuthwa konsekonse? Balam!

    1. u r wasting your time if u think Peter will go so soon, maybe you will be the first one before him cos dat man has got more than nine lives

  9. Uyudi adzipita walalatakokwana nde mukamati rip ndikudabwa tichenjere kulimoto kukanthuko!then he is nxt i dnt know hu me u

  10. Munyoza mtembo bwanji,anakuberani chani,muleka kumalimbana ndi chair Lady wa cashgate mmamuopa eti,anali a MP achipani cha UDF poyamba,ife tinkawakonda,Ambuye waakondetsa,kuweruza kuli kwa mwini wake,nawe lako likadzakwana uzaweruzidwa

  11. BREAKING NEWS: The ruling Democratic Progressive Party (DPP) Secretary General Ecklen Kudontoni has died after being involved in an accident enroute to Kasungu from Lilongwe. DPP spokesperson Francis Kasaila said Kudontoni was involved in an accident around Bua area and his body has been taken to Kamuzu Central Hospital. The cause of the accident is not yet known.But unconfirmed eyewitness reports indicate that the front tyre of his Toyota Fortuner vehicle burst before it rolled.

  12. Pepani akubanja la akudontoni tikuziwa muli pachitsoni chachikuli pangodzi yomwe yakugwerani. Yang’anani kwa yehova mwini zonse ndiyemwe amathondoza wotsweka mntima.

  13. sorry
    ma members ena a DPP mtengelepo mphunziro makamaka iwe pitala kumaliro supita kumangokhalira kugula magalimoto ndalama zake zomwezi za anthu iwe umangothapako oooohooooo!…siku ndi limodzi

  14. amati chisilu chili ndi mwini maliro sasekana muzaziona chikazakugwelani dziwani kuti munthuyu ali ndi abale ndi ana so dont talk too much

    1. maliro ndi ndale ndizinthu ziwiri zosiyana ziwa kuti pali achibale ena akuwona zomwe zikulembedwazi samala ndimayakhulidwe poti suziwa chobwela mmawa

    1. Ana Apansi Pa Nyanja Sasoweka Zoyankhula Zawo, Remember dat “Moto Umapita Komwe Kwatsala Ntchire ” Get Ready.

  15. This politician’s if their doing their political they don’t think they can suddenly death like this but imfa sikusankha ilibe time kodomton samaembekezela angafele pa msewu phumziro kwa osalafe mzimu wake ukause mumtendele ngati mkwamtendele

    1. Hahaha kundipweteka kwachiani athu adpp inu mumasakelera zopusanzo aziba sokho watha ine ndidzisowa magetsi kuchipatala ndizikalipira??? Ndiye ukufuna asafe iwe annie?? Kapena iwe siudzafa ingokoza mtima wako aise osati uzipanga against ine,

    2. Ngati arephera kumangitsa chipatala kumchinji uku mpaka muthu wamba ngati ine kumangitsa ekha komano kuthamangira kukadura liboni basi kkkkkkkkkiest

  16. Sibwino kunyoza nzako pathu sipa dziko , mwatibela zambili kauseni ndi ntendele ngati kuli kotheka

  17. This 2016 eeeesh ayi… am speechless! …Watilanda Grace Chinga, Izeki, Zakaria, Mbendera, Mtafu, Chakuamba, Wame taika dzanazanalii lero ndi Hon.Kudontoni! mmmm..Kwathu si padziko koma ngodala okhawo amwalira ali mwa Ambuye coz zinazonse nchabe…. R.I.P

Comments are closed.