Zanu zimenezo: boma linyanyala a Malawi ogwidwa mu dziko la South Africa

Advertisement
Lindela RSA

A Malawi onse amene anagwidwa mu dziko la South Africa kamba kopita mu dzikomo opanda chilolezo ndipo akusungidwa pa malo a Lindela kudikila kubwela mu dziko lino ayiwale kuti abwela msanga.

Izi zadziwika pamene a boma anena kuti alibe ndalama zokawatenga a Malawi amene akusungidwa ku malo a Lindela.

Lindela RSA
Malawians at Lindela will not be helped.

“Mu ndondomeko ya boma ya chaka chino munalibe ma dongosolo amenewo, ndipo boma likuvutika kupeza ndalama. Silingaseweletse ndalama kukawatenga anthu amenewo,” anatelo mkulu wina ogwila ku unduna woona za maubale ndi maiko ena.

Mkuluyu anaulula kwa Malawi24 kuti a boma aganiza zoleka kutenga a Malawi amene anagwidwa mu dziko la South Africa ati Kamba izi zikuthela dziko lino ndalama.

Koma poyankhulapo, nduna yoona za maubale ndi maiko ena, a Francis Kasaila, anati pa lamulo boma la Malawi silikuyenela kukawatenga a Malawi kumeneko.

“Si ife tinawagwila, linawagwila ndi dziko la South Africa. Amene anawagwilawo ndi amene akuyenela kuti athandize anthu otelewa kubwelela kwawo,” anatelo a Kasaila.

Iwo anaonjezelapo kuti malamulo a pa dziko lapansi amafotokoza momveka kuti dziko limene lagwila anthu ndilo likuyenela kuwatumiza kwawo.

Amalawi oposa chikwi (1000) akusungidwa pa malo a Lindela amene anthu amanena kuti amakhala ngati ndende ndipo kuli nkhanza zosiyanasiyana kuphatikizapo kumenyedwa.

Advertisement

480 Comments

  1. Kukhala kulindera ndikumalawi nde zikusiyana pati? Zonse ndi ndende basi bolanso Ku lindera magesi 24hrs samathima chakudya chaulere mulungu awatsogolera amalawi onse Ali Ku linderawo ndipo atuluka ndikubweleranso dziko muno

  2. Hahagaha ife tili kuno m’pakana zofuna zathu zitapezeka akatigwila timakathamanga kulindelako kwa myezi 4 osatiso 6 ayi ndipo tikumatuluka dziko lamalawi tikuyembekeza kuzagwilisa ntchito ma U S A posachedwapa ngati mukulephela kuthandiza okolamba amasiye ndi osauka ndiye mungatikwanise ife omwe tili kuno pepeni musatilangulise posakhala ife

  3. Chomwe ndaona mu zaka zonse ndikukula nkumakhala pakati pa a Malawi amzanga…
    1. Mmalawi amakondwa mzake akamavutika.
    2. Mmalawi ndimunthu wodzikonda koposa mitundu yonse ya mu Africa
    3. Zimakhala zomvetsa chisoni kuona mmene a Malawi amasankhirana mitundu kuno Ku SA.

    I have read and scrutinised most of the comments here. Mmmmm am completely out of words kuona enanu zomwe mukulemba…kusonyeza kuti you are indeed pure images of the devil himself. How can you be happy pamene amzanu akudutsa nyengo zowawa……mxiiiiiii.

  4. Zoonadi khazikitsani mitima pansi mutuluka guys.God be with u,you do alot here in mw but mw does not appreciate u.many houses eg here in mzimba are build by rand which comprements govt efforts.KEEP UP!

  5. Or Muzinena Active Ndi Passive Voice Anuwo Ku Malawiko Koma Ife Johnz Tidaimva Kukoma Ndipo Mwinanso Tigula Mzika Konkuno.Tikuthawa Chi Trump Chilikumenekocho,vuto La Magetsi,njala,umphawi,vuto La Madzi Ndi Zina Zimene Zili Kumenekozo.Ubwino Sitili Kundende Mwamvatu?

  6. Ife Ndiye Tikudikira Ma Passport Tikupita Konko.Tikuthawa Mavuto Ali Ku Malawiwa.Madzi,magetsi,chakudya Chikuvuta Plus Apo Mwaigwetsanso Ndalama Yathu.Mpaka Mwapanga K2000 Yogwirana Ena Akuitcha Chi Trump Ndiye Pali Nzeru Pamenepa?Go Konko Eya Ee Go Konko Tikaone Kusintha!

  7. Ife Ndiye Tikudikira Ma Passport Tikupita Konko.Tikuthawa Mavuto Ali Ku Malawiwa.Madzi,magetsi,chakudya Chikuvuta Plus Apo Mwaigwetsanso Ndalama Yathu.Mpaka Mwapanga K2000 Yogwirana Ena Akuitcha Chi Trump Ndiye Pali Nzeru Pamenepa?Go Konko Eya Ee Go Konko Tikaone Kusintha!

  8. Busy talking about other’s people’s status forgetting your own the the question is why people r running away from malawi provide job then no one shall run u dot knw Lindela and u dot even know south Africa but busy writing kkkkkk God is not a Man he is with us here and one day those people Amene Aliku Lindela mulungu azawayankha

  9. we are here bcz our country malawi its tooo poor … the whole country its rural area … The money im geting here its over 100 000 mk per month … Just imagine who is recieving this money per month in nyasa goverment ? We wont come bak untl get citzen of sa ….

  10. Mbuzi zimenezo kakaka kwa eni,kuthawa kulima basi,mmalo momatukula dziko lao zikumakanilira Ku maiko aweni,nde mmalo moti boma liyang’ane kuti mavuti aikuno monga njala,kuzimazima kwa magetsi ndizina asova bwanji zoona ndalama azionongera mbuzi zimenezo? Zachamba zimenezo asiyeni Kaye abakhaula kumeneko kuno azikazi ndi makolo ao samathandiza mkosi isaaaaaa

  11. Awuzeni abomawo kuti Iwowo siMulungu kuti angasinthe nyengo zawomwe akuvutika kamba kogwidwawo ayi. Mwini zonse atafuna mzotheka kukafika msanga kutsutsana ndimaganizo awowo. Chilichonse chimadika nthawi, ndipo nthawiyi ikakwana sipakhalanso kufunsa munthu kuboma.

  12. Awuzeni abomawo kuti Iwowo siMulungu kuti angasinthe nyengo zawomwe akuvutika kamba kogwidwawo ayi. Mwini zonse atafuna mzotheka kukafika msanga kutsutsana ndimaganizo awowo. Chilichonse chimadika nthawi, ndipo nthawiyi ikakwana sipakhalanso kufunsa munthu kuboma.

  13. Time will tell ; God will take care of you… You left here for the sake of your families. Heavens knows that love is lost,,,,, our leaders are asleep- …. And their failure is a chance for someone. Let me tell all those affected that we are more than there… We are not where we were … Im praying for God’s kingdom to come just like how Jesus christ taught us to….. We are in pain…pain and pain. But i know time will tell.

  14. inu a news24 ndiye mbuli zenizeni, muzifufuza kaye musanalembe nyasi zanuzo mwanva, talembani za kudula kwa katundu,talembani za njala,talembani zifukwa zomwe anthu akusiyila warm heart of Africa mkumapita ku maiko ena, stop posting nyasi zanuzo pliz

  15. Ndipachimake kusathandiza anthu amene anapita ku south africa kukakhwila ntchito angathandize bwanji pamene dziko la malawi likwamvuta kuyendetsa pomwe mangetsi. Malawi yonse madzi omvutkila tingoti bomali lalemphela kuyang’anila anthu ake amene ali m’mayiko mwina limodzi ndi dziko mwakemomwe utsongoleli muli bwino ndisekeko pang’ono kkkkkkkkkkk chosangalatsa ndi cha kuti dziko la SA linatha kumvetsa kuti utsongoleli ulipanowu umapangila nganza zika zke ndiye pano amati akangwila akumangongala miyezi yochepa ndi kumutulutsa ndipo akumamutenga ndi kukamusiya pamene anamu ngwilila mulungu adalitse dziko la south Africa

  16. A malawi24 mungomuuza uyo dzanja limodzi kut adzipanga zake ife amene tilikuno ku SA sindefe abale ake angozitaya ndalama za bomazo angopitira ku chipatala akakozere dzanja lakelo and tell him fuuuuck chifukwa ife tikudya money pano pa Mzansi.

  17. Osawatenga amenewo palibe yemwe anafa ndi umphawi ife timakhala ku malawi kokuno mpaka atipangira k2000 inu munathawa mitsonkho ndiye boma lizitenga mitsonko yathu azikanyamula alesi wothawa nsonkho.

  18. Malawi ndi prison kale payokha, kukhala mmalawi ndi kulimba mtima now adays, no electricity, no water, no jobs ,heavy taxes. poor leadership,

  19. Koma ukanaona Ma galimoto amene anzako akuyendela kuno and disember iliyonse akumabwela kuzaona pa den sibwezi ukukamba manyiwo

  20. Better to be in lindela lather than to be in Malawi after 120days am out of lindela may be u don’t know and its the people working in RSA who bring money to Malawi I think some pole can agree with me.Ask mukhuru bank we tell u more

  21. Dzikochitikaso kuno Ku Tanzania amalawi okwana 270 akusungidwa Ku kisutu .chifukwa chiti alibe chilorezo chonkhalira mudziko laeni TZ.zonsezi zikubwela kamba ka mavuto a mudziko lanthu la mmalawi .kuonjelapo ena omwe ali mukistumu ana ang’oang’ono.

  22. The Problem with Africans is that we like things which a complete…
    What iam Trying to say is that we like things which our friends have laboured for, and calling good place UK and S.Africa that ther is greener pasture.

  23. Can u guyz tell me y most of pple wen they realesed from lindela amabwelabe kuno? ….wat i knw is simulandu kupezeka dziko laweni ulibe chilolezo thats y amangowasunga nkudzawatulusa…..tell gvt dat tikudziwa kale kut sangathe kutitumizila transport nanga ngat mages,madzi nd ndalama yavutila ku MW ko………musadzivute after some months we wll b back to our works sitidanda……..pali mtendele mavuto amakhalanso pomwepo……koma to stay in MW without working its better to come here start quallring wth police.

  24. Mwatopako kumalawiko? Mene tilili kunoko tonse tibwele kumalawiko muzizatidyesa kapena mutipasa zintchito kupusa basi mmmmm mwapangaso 2000 imozi ndiye tibwereko mpaka mu pangasotu 10,000 kwacha, mutisiye tikatopa mutiona tikubwerako,malo mothesa njala mukulimbana ndi anthu imwe akuyesesa kuthandiza azibale awo ( tilii kunoko chifukwa chosowa zochita kumalawiko)

  25. what a stupid government,yes u deny us today but come 2019 u wili need us! i’m telling you i can not compare Lindera nd malawi kuli bwino kusakha lindera ndi malo abwino kusiyana ndkumazuzika mu dxiko lako lomwe .lindera si prison ai musamanamizane ngat kulamulila kwakuvutani kuli bwino kusiya anzanu ena alamulilepo,nanga ndi fundo zautsongoleri izi

  26. Evn though you defamme us fo being in south africa just wait u wl how good n wise we r mukakukutakuta chimangacho mulekaa kkkkkkkkkkkkkkklllkkk ine pano sindizabweraso ku iguputoko

  27. boma liyenera kuganizapo bwino….coz lindera simalo abwino …..ngakhale ameti sikundende….komabe malowa siabwino …..zakudya.,pogona, moyo wake siwabwino coz they take us like animals once we are in there………4 month inside it’s not a joke…aganizilene anthu ali ku lindera….
    if not tizigwidwa ..ndikukakhalako 120 days inside…ndikutuluka koma mudziwe kuti sindizabweranso coz chikhala chizolowezi..choti ndikagwidwa after 120days ndikatuluka till atandipasa mapepala..

  28. Patumbo panu akumipando inu mukutitopesa osamakhamba za chi k2000 cho bwanji shupit agalu lindera si zomba prison ndimalo awino kulimbe kulima osati kumalawi ku prison kulima chimanga ,kabichi koma osaya kumakokhutisa akumipandowo shupit talema nazo sopano tinukha maginatu

  29. I ws there for 3months, Mulungu ndiwankulu akutiteteza. Kumalawi ulova wakula ndeno kuno timapezako zofuna zathu timasamalira mabanja kmaso kuthandiza azibale. Boma la Malawi nkhanza zaonjeza. Mr Ibu aganize bhobho

  30. Ndipo akanaziwa mene amatikondela ma bwana a kuno sakananene ndife ma hard work kuno ukamatsazika kuti ukupita kaya kumudzi bwana kudandaula, lindela it’s not prison like chichiri

  31. Kusaganiza kwa kwa atsogoleli adziko koma mutakhala pansi kuganiza ndalama zomwe timalowesa m’dzikomo muzaziwa kuti kupanda ife bwenzi Malawi pano atapitirira pa level yomwe Zimbabwe ili koma chifukwa chakuti m’boma mulibe kanthu mwabamo kale nde mukuona ngati ndi nzeru kutero koma cool we are with our money we didn’t ask the gonverment to provide us with something to come here so keep ur dirty mouth shut ! N leave us alone we have our own means.

  32. Paja Walemba Iwee Malo Mobibila Kumusi Umabibila Mkamwa eti……Hu Told u Kt Lindera ndi Prison…..Kudzuka Mamawa zoona nnsnkhu onsewo Kumalemba zopeperazo……?Son Of The Devil Osamangokukutika Ndi Umphawi Ulikwanuwo Bwanji……Tayang’ana Pamene Wagonapo Shamee Mwana Wahule Bvuto Ndi Makolo Ako Kuti Unabadwila Mtoilet mkana Always Umalemba Zopanda Pake

  33. Cen malekwa how many degrees u have? Bcs in mw as of now Zimbabwe two teachers is nafing alonda , unless idont know better explanation to , quite better here than zim two

  34. Akulu akulu zisiyeni izo nziwanthu zotsalira nkulingalira. Amangomva zoti Lindela samadziwa tanthawuzo lake. Amenewo ndi anthu omwe akuvutitsa anthu mdziko lawo lomwe. Munthu wakafunafuna zochita…..akuti akufuna ndalama zaboma….boma lake liti? Is there any Government in Malawi? Dziko loyendetsedwa nzitsiru zokha zokha tsiku ndi tsiku nkhani yake ndiyandalama zobedwa m’boma while mukuti mulipo aAnt-Corruption Bureau. Ndichani chanzeru boma lanulo likukuchitirani? Kuzimitsa magetsi tsiku ndi tsiku,mwezi ukatha akukupatsani bill sizinaoneke. Bill yamagetsi owunikira mnyumba mwanu kuMalawiko kukwera kuposa bill yamagetsi omwe akugwiritsa ntchito factory ku South Africa mukulimbana nakoko. Kamba kakupusa kwanuko mmangotsutsa zirizonse,zabwino zoyipa simutha kusiyanitsa mathero ake ndi amene mukuwaonawo dziko lanu lomwe kumazunzidwa kusowa madzi amene oti mumwe.
    Zimvere chisoni Iwe wangotambalala kuMalawiko kudikira kupangiridwa,uti ukudalira Boma …..uzingodikirabe choncho moyo winawo mwina zidzakuyendera…..

  35. W@ ever u can sae makes no difference to us!! Malawi will remain the same, SA will be as it z!! Being in Mw it doesn’t mean ndiwe olephera!O else To b in Jonz it doesn’t mean kut ndiwe ovaya! Zongofunika ndikulimbikira baxi, some they r making it ku Mw n some in Jonzi..so there z no need to b pointing fingers or kumatukwanizana just bcz ur in Jonzi or Mw…..HOME Z BEST✌

  36. Atsogoleli Aku Malawi ngakhale mukamakhala mumazicha kutindinuyo atsogoleli kapunzilene kwa Mr president Obama zautsogoleli,mtsogoleli Ku Malawiko anapuma acheya anali mtsogoleli osati zamowaziiii

  37. Nkutheka ma Born Free simukudziwa;
    Dr H Kamuzu Banda anali Katakwe!

    ¤ Ku University timaphunzira Ulere
    ¤ Ku NRC, Sciences, ulere koma nkhuku ndi Tea wa Mkaka lololo
    ¤ Ana a School, Bus amakwera Half fare
    ¤ Odwala amapasidwa ma Warrant kukwera Express
    ¤ Ana Onyentchera amalandira Soya ndi Mkaka
    ¤ Mu Zipatala zonse munali mankhwala okwanira.
    ¤ Pa Nyanja ya Malawi, panali ma Sitima oposa atatu, Ufulu, Mtendere, Ilala, Nkhwazi etc
    ¤ Mpira National Team timawina.
    ¤ Ku Army kunali nkhokwe ya Beef.
    A Police amalandira “Ration” Nyemba zoyera, Chimanga etc
    ¤ Magetsi osathima mwa chisawawa.
    ¤ Mu ma ADMARC munali Chimanga, Ntedza, Nyemba, zotchipa.
    ¤ One Kwacha was equal to One Rand, Dollar sinali nkhani.
    ….
    Funso nkumati; Kodi zonsezi, zidanka kuti?
    ….
    Ndikuona Kamuzu akutifunsa kuti; “Mululiranji?”

  38. Hahaha wanyanyalayo ndendani ifekuno timasangalala…ndiposo timataya nthawi yanthu kumakapangitsa mapasipoti azitigwila ndebwino timasamba madzi amoto timadya bwino amatitulatso …tikatha miyezi…itatu.. Osati dziko lauphawi dziko pakana 2ooo. Kwacha . Km..ku.south africa ndi . 2oo.basi …PEPANI MUZIPANGA ZANU A.MALAWI —24 IFEZIKUYENDA BY BAY

  39. Boma lusowa ndalama zogula mankhwala mzipatala,wina ayi akufuna transport yokamutenga ku lindela,,,ife mungotibweretserako ma bulangete if possible….

  40. Ndipo ineso ndakhalako kulindelako atandigwira patatha miyezi itatu anadisiya pano ndikupitiriza kugwira nchito yanga ndiye mukanena zaku lindela sikundende anthu amakhala mwa ufulu chokudya chokwanila pogona pabwino pa bed madzi osamba otentha abwino zimangovuta kuti sulandilako ndalama ndiye inu zichedwani ndi kukamba zakulindela abale onse omwe mpaka pano adakali komwekobe tingowapemherela kuti matsiku awo akakwana awatulutse

  41. Iwe wa Malawi 24 nthawi zonse umangobweleza za ogwidwa ku Theba vuto lako ndi chani? Osamakamba za corruption, blackout ndi njala zili ku Malawi kwathuko bwanji? Aliyense Mulungu anamudalitsa mosiyana. Ena akuchita bwino kumudzi komko, ena zinawakanika kumudziko anadalisidwa atabwera kuno. Ena business ikuwayendela koma kwathuko kukhulupilila ufiti too much a business wo ambiri ndi okhwima. Ndiye amene tili kuno tinabwera ndi cholinga chopungula umphawi wathu. Sikufuna kusiya makolo ndi abwenzi kuzakhala kutali kuno. Kutali komkuno anzeru akuthandiza abale awo. Ndiye ena mukukomenta za fodya kunyonza anthu omwe ali ku Joni chonsecho mukuvutika kumudziko. Mzoona kuti nonse mukunyoza apa muli pa ntchito zabwino? Mumalandila zingati? Muli ndi pokhala? Si ma tenant inu nyumba zakenso za denga la udzu. Ena kumudzi komko ndi ma tenant a anthu omwe ali kuno. Ena ndi ma driver a ma minibus omwe eni ake ali kuno. Kholo lina lili ndi ana 7 koma mwana mmodzi yemwe ali kuno ndiye walimangila nyumba, ndi yemwe akuligulila chakudya. Iwe ukunyoza apa mayi ako akufumbwa ndi njala chitsiru cha munthu. Ku Lindera si ku ndende munthu umakhala momasuka koma chilungamo ndi choti pamene uli komko chithandizo ndi masomphenya zimayima kaye. Ndiye musamathe mau umphawi womwe ukukulankhulisani zovundawo ndi womwe tinathawa kumudziko ndipo anzeru Mulungu watikweza olo titabwela kuzakhala enanu sitingafanane tapanga zazikulu zomwe sitimazilota tili kumudziko. Enanu ndi kuwawidwa mtima kuti muzafa muli chimodzimodzi.

    1. Ndapangabo business Ku malawiko after my brother send me 10thousand rand,nothing, pakalipano he wasn’t gv up on me he gv me again only 3000 to do my own business, panopa ndimuchallanger ameneyo ndingamulile ndalama za chaka chonse,mpamba waine osaduka.Kamuzu anali mafia timadyetsana tokha osati zalero zongobela anthu osaukazi,ine panopa ndikuyiziwa yanga 40million sikuti ndikunyada kapena kuwuza gulu aa,koma kuphweteka mtima ndi ndale za kumalawi kwathuko

  42. Kundende ndi dziko la malawi zikusiyana pati bolaso kundendeko mbalame yochenjera yimagwidwa mlomo khuluku amadya kamozi buy your expensive cars now we are stupid pipo coz we gave u vote pls give my vote back

  43. Dziko la malawi liyenera kupempha dziko la SA kuti a malawi apatsimdwe chilolezo chokhala dzikomo ngati momwe a zimbabwe akupagira samvutika amakhala ndi mapepala

  44. Lindela iz a nyc place than Some of other places in malawi evn lyf iz not of that hard lyk the way it iz there.Long live malawi ,see u if God allow its beter to suffer in a foreighn country rather than die wth poverty in ur own home land

  45. Amalawi24 mungolemba zopusa kusowa nkhani eti, and enanu mukhalira yomweyo kudalira boma likupatseni coupon ya subsidy. Pamene ife titha kugula fertilizer at any price.

  46. Musatitenge inde ndalamayo gulilani chimanga, Anthu akukomokelani

  47. ulibe ulemu. ndiiwe opangitsa manyazi. zeru za chibadwidwe zako nzoperewera .udakuladi mwauphawi nyasaland chilikuti chako chankaka ndiuchi chikondi. ndafuna kukutsikimizira mopanda manyazi kuti uchidziwe chilungamo.zako zeru kuyambila lero udziwe kuti ndimpalabwazi.

  48. Iii mukuchedwa kaya ife kuno wankaka evry day magets 1-90 akungoyakabe mavuto athu ndi anu sangafanane, munaiwala kalekale zot dziko limakhala nd magetsi, kulindela phwanya ndyosamba nyama,mazila, bred mix ma fruits abho abho kumangonenepa maganyu diwu diwu pomwe inu mukungokanda palibe munganyadile kmeneko dziko linavuta limenelo mkaka unauma watsala nd tsabola ekhaekha pepan ndithu!

  49. Machende ako amene walembawe wayesa kulindela nd kuchichili kongokhalira kudya nyemba ukuganiza kut 2000 ugakulire chani galu iwe ife kuno R50 kunya mokwana bwinoso olo itakhala one week imakwana bas ndpo olo boma litapanda kuchtapo ka2 atuluka bas ubwno wake sakuvutka kudya chimoz moz kuposa iweso amene uli kumalawi kape iwe mbuli wachabe chabe trasport yobwelera kuno ukuizwa iwe ife tmaipeza 2weeks ndkuyamba kupeza maproft ndpo kaya umagwla tchito yaj kumalawiko kuno olo ndtamaseta khalamba stngafanane olo pang’ono pomaliza ndngot pantumbo pako nd amene anaku2mawo!

  50. c`nt wait 4 2019 wina adzabwele wandale ndinkhani zake zopusu kti timu votere azandinva ndinthu,let mi tel u my brotherz N` sister hold tight the God of Israel`s hiz nt far 4rm whr ur.

  51. Being in lindela is much better than being in Mw according to finance. Can’t u c zat u r being punished in ur own country? Ha ha haaaa! Simmene ikukomera Rand kuno. Nde ndili mu Zansi mwenimwenimo, zip ur mouth kkkkkk

  52. akunama anthu kugwidwa sanayambe lero ndipo palibe nkhani yachilendo kapena yopatsa mantha lindela simalo ngati ku chichiri prison kkkkkk ndimalo abwino kuposa ku mount soche tangoganiza kudya bwino ngati ukudya ndi president, pogona pa booh tea wa cremora, kudya lachine paron srice paron ,kumwa amasi full time tsopano iwe malawi 24 samala ngati ukulephera kusamala anthu amene ali kumudziko ndiye ife kubwera uzakwanitsa? Shiii!’ unthin fweenthu!?

  53. akunama anthu kugwidwa sanayambe lero ndipo palibe nkhani yachilendo kapena yopatsa mantha lindela simalo ngati ku chichiri prison kkkkkk ndimalo abwino kuposa ku mount soche tangoganiza kudya bwino ngati ukudya ndi president, pogona pa booh tea wa cremora, kudya lachine paron srice paron ,kumwa amasi full time tsopano iwe malawi 24 samala ngati ukulephera kusamala anthu amene ali kumudziko ndiye ife kubwera uzakwanitsa?

  54. lindela is the same like chancellor collage n u can’t blv that is a place to keep the foreigners, I was there 2008 n I can tell you anything about that place not kumangokamba zopusa zanuzo,instead of talking about Peter kuti akupatseni chimanga muzidya,busy ndi ife kuno, chitani manyazi angoni satha onse

  55. Komanso kwaonse amene anena zimenezo amapephela akapena amauluka kulindelako amakuziwa bwino bwino mulindi ana inukoma samalani makamwa anuo polankhulapo

  56. n the goodness is that,ppl r staying in lindela for few months then they are sending them bck to their places again, we don’t care about government of Malawi after treating us like foreigners in our own country, we will be here until God finish his plans in our lives.

  57. chomwe mungadziwe iñu mbuli za xool źonse muli mipando ndizitsulu źa akazitape apà mw pa mpanje SA ndiziko lomwe lili ndi anthu obwera ochuluķa Nigeria liĺi ndi anthu osachepera 13 million , Zimbabwe osakàmba ndi ena otero kma zitinamve źopusa ngti izi ndalama sàmaliżira konko amatumiza katundu mumatenga tàx so what’s ur problem ur naayiii

    1. Tax yake iti yomwe boma limatolera pa anthu amene popeza katundu amabweretsa mozemba mma truck.. osamangodana ndboma mpa zopusa zomwe

    2. mmmmm shameless ngati ma track amadusa mwamba chabwino kma ngati ndi museu ndye ukufuna unene chani athese katangare ma boarder osati zopunsà ukuyikila umbonizo u just wear tay bt u nayiii also

  58. Anthu Apanda nzeru amangonyoza, Upita Ku Jon anapita ndi ndrama ya boma, m,malo mugula mankhwara, m,malo mogula chimanga akamutenge bwampini Ku Jon, Kuyambila muja kutengedwa sanalapebe, alekeni kuti wena atengere phunzilo, chifukwa anthu opusawa achuluka

  59. Thts no fair… Lindela its not a place to be … Thy government must do sumthng to my fellow malawian. We know tht thy government have no money but the should do sumthng. Thts all we need.

  60. ILIBENAZO TCHITO SITIMA DYAKWANU NDIPO SITINA BWELELE NDILAMA ZANU. Kkkkkk kod boma lamalaw Lima ganizila anthu.kkkk mukule phele kuthandiza amene alikonko ndiye mukhanthandize amend Ali Ku south Africa. Ngat muli ndichinthandizo nthandizani amend alikomko Ku Malaw .

  61. malawi sidzathekaso bas akaona mavuto a dziko magetsi,water and difference thing akuona ngat atluza ndalama zambiri,asiyeni atuluka after 6 month komaso choti adziwe ku lindela ndi dziko lamalawi bola komwekuno ku lindela .momot mupeze plan kt magetsi madzi akuvuta kod tipange bwanji, malawi is vry poorlest than south africa.

  62. amenewo asovetu…. their plan A was to go there without legal documentation… before going they were to have plan B of what they would do if A failed and they didn’t….. bringing them back is not a solution… let them solve it there ena asazapangeso…… timadana nzopusatu ife__ error yama local civilians isamagwe ngat nd vuto LA boma….. akhale konko amenewo…,…

    1. your right victor….. but sometimes we really have to do things the right way no matter how long or tough they be..,.. if not then we only end up reapeting such mistakes

    2. Khala chete iwe ,angalowe mu shop kukagula chovala cha 3500r,even mamuna wakoyo,ngati uli okwatiwa,kudalira kudya matemba basi oti anafa 4months ago.Malawi sazasitha,zaine pano zikuyenda,ndagwidwapo 3tyms,anzanga omwe ndimaphunzila nawo kusecondary pano ndimabwana koma koma zaine amagwada paine sangadutse even yiweyo ngati uli pantchito salary yakoyo ndindalama za tyre ya galimoto yanga.

    3. you dont sound literate…. to me you sound illiterate that’s why you can’t even know if am a male or female by studying what I jus wrot…. old school did you know good…. kma BG up to u fo making it in life…..PEACE

  63. Ndipo ine i can agree with boma osawathandiza amenewo ayi akuyesa boma lili ndi ndalama zopangira zibwaba et mesa pangotha miyezi yochepa anakawatengako

  64. I don’t know if this gvnment will ever get the votes though they are forgeting one thing that once all the guys have been deported here criminal cases is gonna be high that even the police are gonna be murderd like lice by thugs

  65. Timakakhala opanda chilolezo bwanji? Passport yanga ndi chilolezo kale,kunodi anasiya kupeleka mapepala,anangoti Amalawi zikhalani,nde amatero kumene kutigwira kutisiya,kuzatigwira nkutisiyanso dzaka nkumatha soap ndi ka ndarama nkumatumizira abale kumudzi zathu kuno pheee.ndikakhala ine nde ndizabwera nkhuku ndi youghat zikazatha komanso akazaseka kfc ndi McDonald.

  66. “Kodi inu mbuli za atolankhani mumalimbani ndi anthu a jozi bwa” osamangokhala mumdimamo ndi ma 2000 kwacha anu” mbuli za atolankhani pa facebook…..

  67. DZIKO LIMAKHALA NDI BANK NOTE YAMAZERO ATATU????? eg: MK2000. AGULUKUNYINDA INU. KHALANI NALO ANIWAKENU MUKUTI DZIKO?????? LIKHALE DZIKO MUNTHU WANJI ANGALITHAWE MKUMAPITA KUCHILENDO???????? TIDZABWERA KUZAKHADZIKIKA PAMENE LIZAFIKE PADZIKO. MAKAMAKA LIKAMADZALAMULIDWA NDI MBULI YOSAPHUNZIRA. OKUBA OPHUNZIRAWA AAAAA MMMMMMMMM ATILANKHULITSA PAKATI. PITILIZANI KUBAKO MPAKANA KWACHA ISINTHIDWA MK75 KU R1. LIMALIZENI TINAKUSIYILANI NDILANU LIMENELO SINANGA MUNALIPHANGILA MWAYIWALA MALEMU KAMUZU ANATI MALAWI NDI WAGULU.

  68. I was following keenly all the coments written here….but my heart has been filled with sorrow and the country was not suppose to be my Malawi. Some of the answer given by government officials if at all its true,are very unacceptable and uttered by those who are absurd. Your busy tellin the nation your tired of them,why are you not tired of stealing their taxes? My bros and sisters world over stay where ever you are…some of these leaders are those that talk to their counterpart to punish us abroad for us to come home and meet the new 2000mt,shame on my Government full of educated savages…..mr president, vice president i knw u better than this but ur kids are bringing u shame……….to my fellow foreigners….nthawi zina kumayenda ndi masophenya mkumakumbuka mavuto mwawasiya kumudzi….gwirani ntchito pezani ma means opezera ma papers ofunika msanga mowa mahule ndi zomwe munkanzisowa ndi umphawiwu muli tazpeza tichitiretu…….mukutichitisa manyazi ka …….. Ana anjoka mukhuzumuketu…

  69. Good to be in Lindela than to be with the so called munthalika a president without any interest on his ppl to hell with Malawi

  70. Funken presedent panyo pamake kod akuganiza kut ntchito anthu akagwira komatoko kwa amake mwina chisilu chamunthu chimunthu chosavinidwa kapena chimshezi kabisa chagaga kumbolo

  71. It’s the government that rescues peopple in troubles .so don’t challenge it.governance changes anytime.xenos

  72. Mmmm ine ndifera konkuno kusiyana kuti ndizikavutika kumalawi asaa chi 2000 chimene chi sikuwonjezera umphawiko kumeneko mmmm koma munthu ameneyu bola mulungu akanangotilanda bas Chifukwa palibe chimene akupangaa

  73. Mumawakonda akamabwera ku Malawiko atasanja nde kumawalipilitsa akatundu awo omwe achitanso kuvutikila kuti amupeze .wina azayese kunena kuti ine wa M R A meaning andilipilitse katundu wanga azaona zosaona boma lakolo lizakuphetsa. Ndichita kubwela nditakonzeka .

  74. Msamayankhule mopu!sa zoti kumalawiko kulinkhondo simudziwa ? Munthu ngati akusowa chokudya kamba ka ulova, now anthu akuzithandiza okha inu mukuyamba nsanje kkkk mukhalira yomweyo

  75. Zoti anthu akungopasidwa chilango chokhala ku Lindela 60
    days mkutulusidwa simudziwa? Boma la South Africa lidadziwa kale kuti kwathu kuno kuli Bwampini yeamwe sangalabadila za anthuwo.

  76. Ndivuto la boma,anthu akuvutika thats why amapita kunjako.Ma passport anakweza mitengo anthu sakukwanisa kupeza akanapanga bwanji?Kuwanyanyala nkulakwa they are Malawians boma liwathandize abwere nsanga!2019 muzawafuna and ndi abale athu muzatifuna…

    1. Eric ma passport tili nawo nkhani yoti tikhale ndi ID yakuno ndiye kuli bwino ndalama imeneyo nditumizile abale anga omwe akufa ndi njala kumalawiko awa akukambawa asiye sakuziwa chomwe ali kodi kuno ukwagwidwa umakapuma kulindera kwa miyezi iwiri kenako akukutulusa kuno sikofera koma akutilera bwino bwanji nanga ali ku maula amamwa tea wa mkaka nanga amasamba kuno kuli ufulutu

  77. news 24 please if u dont have something to write just have time to fuck you wife ur so full of shit marete awena

  78. Too much cashget our nation malawi we r voting a fter 5.yrz but nothing is changing it shows poor leader ship even members of parliament are fool of shit instead of to help pple voted for they dont care only that cheating in there minds nonsense God will punish u it iz better not to vote stupid

  79. Amene amakomenta zautsiruwo ndiakumangochi.boma lakuti lingakwanitse kuthandiza anthu Osaka ngati Malawi pa nkhani ya kujoni?apapa boma sunalakwitse

  80. It sms lyk u the malawi 24 u dont knw anythng.in SA they can catch even u hv a passport .they respct you when yo pspt is valid.bt whn u reach 30 days whoooooooo!

    1. Ali pantchito Ku 24news koma akati atchena ndekuti analowa pep store,boma likulephela kuthetsa njala,plan b kunamizila za kulindela matchende ake Mr IBU yo pamodzi ndi boma lakelo

  81. KOMA PAMENEPO MUKUONA NGATI ANTHUWO AVUTIKA MACHENDE ANU NOSE AMENE MAPANGA MA OGANISSEE ANTHU ZIKO LINA IFE TILI KUNO PAKA PAKA. Sitigwigwa ige motherfuckes all mambers

  82. Ngakhale ine sindinakhaleko ku Lindera koma ndimamva kut Lindera siilingat ndende.koma ndichinthu chopweteka kwambri popeza pochoka kwathu kumalawi ndi timati mwina tikayetse mwayi,soka ilo mkufikira mmanja,no one can get happy about this.To those talking shit to your friends attaked and kept in Lindera area,how do you understand if two or three of you coming here in SAC and just only you attaked by government of southafrica?please guyz when you want talking something just think very well to keep playing together.there are malawians we also malawians how do we talking that?ngat tisakumverana chisoni tokhatokha muno ndye moyenda mukuganiza kt,makalade,maxhoza kapena mazula angamvere chisoni?mmmmm that is not good life tizipempha mulungu awathandize anzathuo,in the name of allah “comfort all families where that people come from renspectively”inshaallah

  83. a boma kwasala ndi kungovomeleza kut mukulephela u songoleli wanu nanu a peter mumazitenga kuphuzila kwambili koma muli mbuzi ya munthu shit fuck all amene mukulakhula zopusazi

  84. Inali lindela zaka zapitazo panopa timaka buka ticket ya Bus nkukatenga anthu b4 beilt bridge bus ija yili empty nanga kumalawi ko ndalama tizitenga kut hahaha

  85. Pano zafika posauzana. Sizodabwitsa boma limeneli ketelo but we still wish you guys to come soon as possible and make other moves back. Doesn’t matter facilities you have at the detention centre what matters most is that people get physicalogically affected in such situations

  86. kodi boma lanuli lika mati lanyanyala muku tantha uzanji popeza ku lindela muku nenako ndiku malo osalala kukhala kuposa ku malawi kuno kulibe kukaku limitsa nyemba nmunda mwawina koma ku dya sinkhani osati mavuto ali kunowa kadziko kaka ng.ono kakuku vutani kukala mulila malawi muku maitenga ngati prot ya gogo anu kuma ti bweletsela chi 2000 chouma tizilowela nacho kuti

  87. Awatumize or asawatumize is the same kumalawi kuli boma ngati kulinzika zokhazokha kkkkkkkkkkk mukuona ngati muli ndi boma? Tangokhalani basi kudikila tsiku la imfa

  88. Bola ndizikhala konkuno kulindela kusiyana ndikuti ndizikayiwona k2000 yogwirana kkkkkkkkk malawiiiiiiiiiiii

  89. Palinjuchi pa uchi,,,mdima uzawathera,azalionabe zuwa.God loves those who struggle to get on top, koz akakwera, azapuma mpweya onyadirisa.

  90. Iiiiiii komaa ulamuliro uwuu ndiye worse kuposa wonse!! Bwanji poyamba paja munawatumizira ma bus!?? ndiye kuti munali musanawerenge lamuloli!?? zikuwonetseratu kuti mitu ili kutsogoloku ndi Mamina eni eni!!

  91. Boma lautsiru la Malawi nanga kutachitika zinofobiya why did rush to help omwe anali kalikonse, if the government was wise enough mukanapanga plan kuthandiza mnzikazi koma inuyo katangale basi your time will xpire ena azalamulila mwina angazamvetse kuti why alot of malawians are coming to south Africa, and what can we do to help not people to go there?

  92. Anthu ake ndi omwewa mumawafuna nthawi yakampeni kuti akuloweseni M’boma muzikaba ndalanda lero nkumati ndalama palibe tizawonana 2019.

  93. Abomanu musazivutise ngati zingateke takangosainani mapepa oti antuwo ife talepela aliyese ayendele yake. Nde muone kuti osewo ndalama zoti afike mumakwawo sizingapezeke? Antuwotu sikuti ndalama zoendela alibe. Koma inu ndinu mulibe. Ndetapitani kukawamasele basi

  94. Anthu akagwidwa ndi boma lomwe lawagwira limayenera kuwatumiza kwawo.If south africa ilibe ndalama to send pipo to their countries they must just stop sangagwile anthu ndiye ati boma la Malawi likatenge anthu ake that’s bullshit leave the government alone they have a lot of problem than to go and take pipo from S.A .south africa is responsible for deportation not malawi or any other country dammit………….

  95. Eta! Amalawi 24h mundiuzilekokwapitiyo kuti payz ifekuno tinabwela ndindalama zathundipo sitisowekela nthandizolililose lochokela kwa injawo chingakhale atigwile azatitulutsa ndipotsotizabwelaso sikuyamba komatsikumariza ayi ndyeiwe pirta muthalika usatengelepo mwayi pauphawi wathu ndi azako omweukugwilizananawoo kodisukuziwa kutkukhala kulindela kulibwino kusiyana ndikukhala kumalawiko popanda chochita ndiyemukamayakhula musamakhalengati mwavulakabudula ndikumayala mbolozili patete muzatikwisa ngati zikolikukanikani kulamula mupeze zinazochita otsati kulimbana ndiathu omwe Ali Ku south Africa samala kuti masiku ako achuluke masimba fokolo

  96. Atandifusa kuti usakhe kokhara pakati pakumalawi ndi kulindela. Ndisakha kulindela ndithu. Kumalawi kulibe koti tingafanizire mwina kujahena ndi chimodzimodzi ndi kumalawi. No water, no power, tingoti everthing. Osaiwalanso no president.mukamanyadira dziko lakumotoli ndimadabwa nanu amalawi omwe ali kulindela akunjoya kuposa ife omwe tikusaver jahena tilimoyo. Asiyeni nkoko nawonso kuno sakufunakonso. NDIKHUMBO LANGA KUTI TANZANIA ILANDE CHIGAWO CHAKU MPOTO, ZAMBIA ITENGE CENTRAL YONSE. MOCAMBIQUE ITENGE SOUTH YONSE. IN SHORT DZIKO LAMALAWI LITHESEDWE.

  97. amene akuti zawozo mumudziwitse kuti alibe umunthu chifukwa amene ali kholo ayenera kungala ndi chisoni ana ake akakhala m’mavuto.Koma akuyenela kudikila chiweludzo padzomwe akupangila osalakwawo.

  98. Tikudziwa kuti inde ndizathu,ngati chikukanikani chimanga,,,, ndiye pali ndege? Akotopa nafe kutisunga amatimasulanso,,inu kumemeko wonani za chimanga,osavutika ndimafana a johnz

  99. Matsiku ano palibe kutumizana ife tilikuno mpaka chakudya chanthu chakuno chizakatha sitikuziwayi kuti tizalowela kuti koma only Allah knows zobwela kumeneko akuziwa ndiwapamwamba mwamba ndipo kuno tikukhala chifukwa cha yomweyo akutisunga ndikutiteteza ndiyomweyo kwayiye ndiye kozabwelela ukuti bwanjiiiiiiiiii

  100. Pali anthu ena mangoyankhulapo apa…..simunadziwe mavuto….mukazaziona pomwe simungazayankhule ma comments osaganizira anzanuwa… #Mulungu_si_James

  101. Pofela salambula mawa ndinu mudzawafuna anthu ake omweo mukuyamba nkunyanyala bwanji osayamba mwaunika chikupangitsa kuti azithawa lokhala lawo kuona poti zanu zidayela kale nde muziti boma simungakhale boma popanda anthufe

  102. Lindela is not Maula or Zomba prison and mukusiya kumapanga zanu koma kumalimbana ndi anthu omwe apita kukazipezela zomwe iwo akufuna,Mungozitayisa nthawi chifukwa anthu omwe mukuwanenawo abadwila komweko koma ndichayani chomwe Boma la Malawi chomwe munawapangira mukufuna basi tizikuyimbilani manja mbuzi

  103. While malawians are being arrested in Tanzania, Malawi high commissioner to Tanzania has said that they have got nothing to do with what is happening since it’s not their business, the question is, do we have leadership in our country? It pains alot once come the elections you go out asking for the votes from the people you are denying today, God will protect all malawians wherever they are looking for something legally to help their families no matter the gvt has rejected them, you are in power today and tomorrow is coming

  104. Or musathandize munayambapo mutathandiza anthu opita ku southAfrica sikoma kwabela basi akabwela bwinomo misonkho anuwo mu ma border basi zisilu za sogoleli kuba basi

  105. The difference between Malawi and Lindela is so huge that being given a choice of place I would go for Lindela.
    The only place similar to Malawi is hell.
    No electricity, Water and worse still heavy tax.
    Oh! Ndinaiwala, akuti ndalamanso yatha mphamvu kukubwera K2000.00, I can’t stay here bro

    1. chikumbutso just cry nduwuphawi wako cuz u cant even manage to process a passport…… mtendele? my foot…..imagine mphuzitsi waku primary ngati iwe who gets chicken change less than 50 pin ma 2000 mk anyowani 25 pa mwexi ndeee uzikati mtendele? kunvetsa chisoni……that money here u get in a week or less

    2. Even RSA has introduced a 500 rand note, its also a sign that their currency is not trading well, america soon will introduce 200 dollar note, its just a sign of end of the world.

    3. At 53 Malawi can’t pay her employees, can’t produce electricity and the most basic thing which we have abundantly; water.
      Tikumakhala 2 weeks without water, am not a snake

    4. #AmwenyeGamakoma did u really look the consequences about all this? i don’t get ur understandings here….do u know how India is struggling now over higher banknote? so u wanna face the same probs?……even euro its on €500 higher banknote but they complain now and then…. the ECB is assessing the fate of the €500 euro banknote, as concerns about its use in money laundering and crime grow and its usefulness for large payments comes into question” adding that “competent authorities increasingly suspect that they are being used for illegal purposes, an argument that we can no longer ignore.” (like all other ECB matters, there appears to be infighting on this issue too, and subsequently another ECB member Yves Mersch stated that the he would like to see “proof that high-denomination notes are used by criminals”). So what, big deal, eliminate it. The people will still have 5, 10, 20, 50, 100 and 200 euro bills right……so if Europeans countries cries over higher banknote who are we?

    5. this changing of note so called K2000 kwacha amene angamvetsetse ndiopita ku schoool inuyo,,ofunika civic education kwa anthu,,omwe mukwagilira ntchitowo,,,Mozambique did the same, zimbabwe also,,,so whatchu talking about?

    6. ngat iwe uli ndi zeru bwanji sunapange magetsi ako amzako azeru mesa amapanga? olo chitsime ulibe umadikira boma likukumbire chitsime? ulesi wako wakupangitsa kuthawawira komwe anuwake analimbika kut afike pamenepo. ukupita wekha akakakugwira udzikat boma likuthandize? bushit. sindisilira any other country than malawi.

    7. #pure_francis masiku i feel so pity with…..i cant stop loughin at u….like really? all that taxi we pays then ur telling we wait the government? the is the one wait to shop ur money as i once ate the money too zitabooka mubomamo…..even pokagula borehole materials the government will still eat ur poor money….with ur money pple are driving BMW and new model audi hammer mkati ….i think tikwenzenso misokho tilemelenso

    8. Kendy#. Running your own problems it’s a race you can never win afana,,,,,kharani kumeneko zithandizeni koma kwanu,,ndikuMalawi basi,,olo utakhara,,zaka 50 uzafunabe,,,kwanu

  106. Mind yr busines olo musawanthandize adayamba atabwela kuzakupephani pakhomo panu? And u pipo mumatidyela masuku pamutu boma limatumiza ma Bases aulere kt akanyamula anthu inu kufika kuja mumalipilitsa fuck u pusy.let them stay Lindela ox nt prison u feel free eat watch tv komanso kusamba pa shower after 90 days they gonna release them out.so dnt tak it 4 granted

  107. Fusek galu wakupempha chithandizo ndani kuti utithandize? Ukachite kunena kuti zanu zimenezo kuti chani? Kukamwa ngati kwambuyakowo,, pamene tinkapanga za passport ndi transport unathandizapo chani? Palibe tokhatokha anthu amuna mpakano zatheka.. Panopo tikuzidalira tokha nde loko usiye we don’t care, u motherfucker” tikuonani 2019 pamodzi ndichimbuye chakocho..

  108. Ubwino wake anthu akumangowatulisa pano ku Lindelako. Kkkk stop wasting your time instead think of how you can build Malawi so that we people can came aback to our warm heart of Africa.

    1. Hahahahaha Bressings usovatu Iwe,ntchito kuba ndalama nde do you think you can build Malawi?Tidakakhalabe Ku dziko la weni kuno.

    2. Blessings, you sounds very stupids. First let teach you how to write your name from Bressings to Blessings.
      Second, I have been in Malawi for more than 26yrs working with NGO’s like Yoneco, Plan Mw, CHHR, Nac and Icelandic Union but I’ve never get K13,000 per day as my earning. Here in SA I get R250 per day which is K13,000.
      So tell me how much money am l earning per month?
      Ndiwe odwala iwe eti?

  109. Chauta ndiwabwino zedi amadyesa mbalame ngakhale sizilima.ndinena ndiinu muli kutheba limbikani gwirani ntchito mozipereka pakutha pazose nkupeza cholowa kumoyo wanu.mulungu akudalitseni

  110. Musamati zawo zimenezo.Ifetu sitibwera kunu ndimsangala ayi koma mamvuto azachuma kudziko lakwathu.Ntchito sizipezeka ndiye apa nkupanga bwanji? Muzitifunira mafuno abwino osati kutikhumudwitsa.Tonsefe kuti tibwerere kumalawi ntchito tikaipeza kuti? If all Malawians decide to back to homecountry what would happen?

  111. Ameneyo ndi pulezidentidi osaganizila anthu ake? Akuganizapo chani pankhaniyi? Chimene angaziwe anthu akuthawa uphawi kumalawiko.

  112. Ukuona ngati Lindela ndi prision ndikuuze akati Lindela means malo odikilira dont talk bwatabwata u blood fucken idiat

  113. OUR God never fail sicholinga chawo koma mavuto amene alikunowa ndiamene akupanisa kunakakhala kt atsogoleri akuno kumalawi amakonda dziko lawo sibwez anthu akumakasaka tchito maiko ena koma akungokhutisa mimba zao ndi ana ao amalawi ankhani nkhani akuvutika

  114. chotimuziwe lfe nde a Malawi mipando yomwe mulipo ndife tikafika muzachoka nose akuna nkinga yankhulani za k2000 osati kumanena kuti zanu zimenezo sikukanika usogoleli kumeneko opusa lnu

  115. Amatuluka munthu kulindela masiku ano, mpaka kuli mitengo nde yiwalani, koma tisamati boma lamalawi tidziti labingu chifukwa boma ndi anthu okhala muzikomo amene ali mdzika zazikolo. Tsopano boma labingu ndilachabe lilibe humanity chomwe limadziwa kupanga ndikukaniza tsogolo la ana kuti atukuke that’s y anapanga passport yao yautsilu ija

  116. Chikakhala kwazako umamwa matzi chikafika kwani chimakula tati asogoleli uthenga wu uwafikile athu anu kuno akuvutika ngati muli ndichifundo chitanipo China chilichose tuana tatin’gono tili Ku jeli zowona

  117. Kwa inu muli kumipando lakhulani m’mene mungathele ,poti ino ndi nthawi yanu yoti mulakhule kaya za nzeru kaya zopanda nzeru,koma choti mudziwe anthu omwe mukuwanyozawo ndiomwe mawa mudzawafune munjila INA yake(2019),Choncho mudzisamala

  118. Tsiku lina liri lonse azatuluka they are not there kuti adaba but they were trying to look their green pasture nde kaya mutinyoza kuti we are struggling in this foreign land we are not shaken as I said God is in control with everyone Malawian who is in South Africa death is every where we can’t run for it.Stop talking like kids.

  119. Guys amene mukundimva ngati muli ku Durban vayani ku Home Affairs ya ku Umbilo mukatenge ma asyllum seeker amiyezi 6 ndipo ulumikizane ndi amene wakupasayo kuti azikupangira renew after 6 month kukudyera pin sikuti unganyenyeke ayi wake up guys united we stand

  120. Boma ndiife popanda ife boma palibe chimenecho mtsogoleri wina aliyense amane adzikhala pampandopo azikumbukira chimenecho mudzandivomeleza mtsogolo muno

  121. Nde zkusyanachan ndkumalawiko pot kukhala kundende yakujon bola kusyana ndamene alikunja kwa ndende kumalawiko pumbavu!

  122. Komaso pano munthu akatha 6 months ali ku lindela akumatulutsidwa kubweleraso kuntchito.zathudi izo.ngati tinakatsanzika ku boma kut mukaona zii tatsikira ku zumaland?tidzabwera tikakwanitsa zomwe tikufuna.

  123. ndipo kukhala kulindera ndibwino kusiyana ndikukhala kumalawi shame on your serf, zikolake liti mpaka K2000 ndalama imodzi, zanga ulikulindera mtendere ulinawo nandizuwa lilikumalawi singagwile

  124. Iweyo wa Malawi24 ungotaya nthawi nkapanga za anthu omwe ali kuno ase tikupanga ndalama and abale anamangidwawo tingowapemphelera kuti akhazikitse mitima pansi coz after six months from the day anagwidwalo azatulutsidwa and Lindela ndi it’s not a prison amadya bwino pogona pabwino MA screen ake ma plasma so go tell your motherfucken so called Government that what happens here it’s for us alone, i have been in Malawi with my license for 2 years moving up and down searching for a job so that i can support my family but all in vain, now guess what you little piece of shit, i came here within 2 months i had a good job with good money when i came back to Malawi 2 months ago even your father did not recognize me coz i have changed, so when you want to talk think why people come here, we only come here for a living motherfucker, and go to hell straight with your Government.

    1. it’s not like we’re happy staying far from home and our relatives and family but we have to survive that’s why we are here and we’re f**kg doing good take note

    2. Kulibe dollar kumeneko musanamizane.baranso kuno ukakhala kuti mutuwako ukuyenda bhobho.muzinena zauhule koma.musazilimbikitse guys paja akujoni olo zitakuvutani koma mumafuna muzionekabe madolo.mumakhalira kuzudzika kumeneko.

    3. Spoon yamnyumba iwe ukudziwa chani zandalama? everything is bad kumalawiko kuyambila madzi, magetsi, currency everything is wrong wrong wrong.

    4. Anthu opanda phundu kumalawi amene anthawira kujoni.ubwino wake kujoninso amakakhala opanda phindunso,kumawatukwana zankabudula iwo kumaseka kenako kulemba post pa Facebook akuti” am feeling fresh” kkkkkkkk abale umbuli.

    5. Komabe olo muthoke mbwelera jonz sinama ine 3months ndinamanga den yaboh ku malawi ndapanga ma biznez osiyanasiyana koma ndimalephera kugula ndi lata lomwe mapepala makoswe anandidyera kamba kosowa vep kumalawi hooo malawi ndilibe naye mawu…anyway pot mthengo ndi mwa njoka ndizabwera

    6. Vele amasimba kayadliwa ngumuntu wobaizayo,konke kuyakishwa.vele niislima nina ngako niyathukwa inidinwi.nisphukuphuku nina.

    7. Mapwala ako Bostings,uli ndichiani iwe ,mpaka udzamwalira sudzapeza galimoto yomwe ndagula Ku Joni kuno,makola anga akusangalala,ndalama ndili nazo panopa nditha kulipira Mr IBU wakoyo,Pita Ku Mangochi sadalira Boma,ndidatengela chitsanzo kwanzangawo,zakumachende basi,pamtumbo pako

    8. osatukawana apaaapaaa,,,,, as long as God got you, ,,go on with your life rather mocking and bosting,,,,,,, so many ways of getting money

  125. Inu atsogoleri a mabank ang’no ang’ono like Mukuru,post office just to mention the few pamodzi ndi ma networks like TNM and airtel try to remind the gov kuti anthu amenewa ndiwofunikira bwanji ku business yanu.tsiku lina ndinamva mkulu wina wa zachuma akuyamikira kuti foreign currency inali bwino chifukwa cha a Malawi okhala kunja maka SA, ndiye pano mukuti mwanyanyala.

  126. Chitsiru chimati kumwamba kulibe mulungu.Ndinu zitsiru aboma anthu apange bwanji kuti apeze zosowa tiona ngati mumayesa kuti kumwamba kulibe mulungu.Ndatopa nanu coz mukuzuza anthu & ndilanda boma bwerani mundimangetu ngati mungakwanitse

  127. Chitsiru chimati kumwamba kulibe mulungu.Ndinu zitsiru aboma anthu apange bwanji kuti apeze zosowa tiona ngati mumayesa kuti kumwamba kulibe mulungu.Ndatopa nanu coz mukuzuza anthu & ndilanda boma bwerani mundimangetu ngati mungakwanitse

    1. zgwira ntchito bwanawe zkuyendera ukuona ngat pot malawi akudutsa m’mavuto anthu ena sakusangalala? olimbika akusangalala koma alesi odalira zopatsidwa ndiomwe mukusokosanu.

  128. kodi iwowo akamapita kumisonkhano ya maiko akunja amatenga ndalama zammatumba awo? mesa ndizamisonkho awanthu akukanidwa panopa.

  129. mulungu ndi amene aziwa zonse, iwo popita kumeneko amafuna akapezeko timaganyu oti athandizire mabanja komaso abale awo kuchoka mdziko lao lino lochepekedwa mzinthu zinali. ( loard show your mercy)

  130. dziko lathu lili pa umphawi wadzaoneni ndie palibeso chifukwa choonongera ndalama anthu samapindulira dziko lino coz amachoka dala opanda ziphaso ndiye akagwidwa azibvuta boma la malawi aiwale zimenezo kaya aziponyedwa mu dzenje zawo samapindulira boma olo abwere nd katundu amazembesa ati kuthawa nsonkho boma silorakwa posapereka thandizo kwa anthu amenewa

    1. Hope sukuziwa zomwe ukulakhula .kamba koti uganize ndi anthu angati omwe boma limawadyesa n ndi mafamily angati omwe amadarila anthu ali kuwulendowa .ngati boma ndilawu mphawi si kamba ka anthu omwe ali ku jonz koma kamba ka ma president anthu omwe amango funa kutukula mabanja awo .

    2. kma ngt mudzipita dala ku dziko la eni opanda chilorezo munya simunat coz kuno kukusowa makhwala zipatala ndye kulibwino ndalamazo kugula mankhwala kusyana ndi kuombola dzitsilu ngt inu zenofodia itavuta boma linapanga spend ndalama zambili kukakutengani nde munathawankupitaso pano mwagwidwaso mufuna thandizo zanu peter sangapange nawo zopusa zanuzo muona mmene mutachitile

    3. Makhwala akusowa coz of what? Edo usanamizike kuti boma lanthu lingasithe olo litapanda kukawatenga anthuwo tizivutikabe bola akawatenge tidziwa kuti ndalama zamisonkho yanthu yathandiza amalawi azanthu kusiyana ndikumasowa makhwala zipatala osadziwa kuti ndalama zathu zapita kuti anthuwo amapita kumeneko kuthawa mavuto know that

    4. kulibwino aziba kusyana ndi kukatenga anthu oti anakawayamba dala mavuto anthu amenewa amazolowera akuthawa kulima afuna azitivuta iya

    5. sagwidwa wopanda pasport okha ayi,even uli ndi paspot amakugwira,tsono ngati umadya nao usatero kumakhala ndintima wa umunthu

    6. Edo Malawi can’t do without people or communities in diaspora thus one of major way when it comes to development. Otherwise without these guys our country would be in much dilapidated state than we’re today. God bless you brother.

    7. zosatheka akanakhala amapindulira boma akanathandizidwa kale coz tikat kuthandiza boma tikutanthauza anapita ndi ma work payment kaya xool or matenda not kungopita kumangozungulira mizikiti ngt agwidwa ali ndi mapaper ogwilira ntchito kapena xool or akulandila ndathizo la chipatala apite ku court ndi ma paperz awo akalisumile boma la sa kut likuwasunga ndende ali osalakwa kma ngt alibe chilichonse awasunge ikakwana nthawi yootcha zinyalala awaotchere konko kunoso asabwere tinalimba kale mitima

    8. olo munditukwane ine siothandiza ayi ngt umakwanisa kutukwana utukwane boma lomwe lalephera kukakutenga lindera not me awa ndimalemba apa anali maganizo anga osat aboma ndye iwe uli busy kutukwana ine mmalo motukwana jacob zuma sindisintha ine kuno zanga zikuyenda bwino ndalama zomwe liononge bomazo ndi misonkho yathu tikamaoda katundu mma shop kuno ku mudzi tanena chomwe umalipasa boma ukabwera ku joni kwakoko nothing pomwe ife each and every day tikupereka msonkho ku boma la malawi

  131. I bet you can’t give APM a news blackout, where will you get your daily bread?, because you make money/sales out of him. You went there/Mount Sochi just to while away time in anticipation of the coming growing season.

  132. Akufuna afe ngati m bale wake ndi KADYA KALISITA kkk kukakhala onse ali ku joni anali m Malawi kulongolola kulipoku kukafika pati kodi nchifukwa chani akuoneka ngati pamipando amakhalilapo zeru za zimai awo ai ndithu chi mtchona chimenechi Mulungu akanangotilandilapo chatikwana

  133. Zilibe kathu choti mudziwe amalawi omwe ali kulindelawo akusangalala kuposa ife amene tili kuno kumudzi manyumba anthu. Iwo sakusowekera madzi ngati ife, sakusowekera magetsi ngati ife. Sakusowa chakudya ngati amalawi omwe ali midzimu. Kodi lino ndiziko lomalinyadira kuti simuwatenga mwachangu? Poti iwo akulira kamba koti atumizidwa ku jahena kuno. Pafika bola galu wakujoni akusangalala kuposa munthu weniweni wakumalawi. Stupid government

  134. Hahaha Lindela is not a prison but waiting area, it’s not like Maula prison munthu amagona pa Bed not pa floor en amawonera Tv so plz the government we will be back home if the government will hv means of create jobs for us it’s not our wish tayesetsa kumudziko kuti tithandidze ma banja ndi azibale athu while kuno kochepa komwe timapedza although we are staying mobera but God is protecting us each en every hr kufa ndithawi so stop criticising us God is the one protecting us here not the government en those who are now struggling at Lindila God himself knows their future not anyone

    1. It’s okey ndibodza koma chomwe mufuna anthu apange nchiyani??? I already said its not our wish to stay here we tried to look for the green pasture at our own yard nde tisiye maganyu athu tidzipita ku Malawi tidzikatani???.Ngati boma silikufuna kuthandidza likhale we are not scared to die as long as we are dying for the truth man sitikuba kuno we are working omwe agwidwao samaba komanso ndalama yomwe itha kuthandidza anthu awa ndi misonkho ya azibale athu I don’t where dd I go wrong man koma lindera it’s not a prison note that

    2. Duma chirwa sionse amakhala movutika, Do u want to tell me kuti onse aliku Malawi amakhala mwamtendere although ndi dziko lawo??? Komanso kuzunzika kwathu we are trying to raise school fee’s for our brothers en sisters including our own families I hope u people mumasangalatsidwa mukamaona anthu akuba

    3. Nanga dziko lako lomwe uzunzike Bola kuzunzika kuno kwa eni .Ine ndiye ndilibe kalikonse koma ndikukharabe bwino opanda chobvuta

    4. man asiyeni amenewo akupwetekesani dzala bola ife kuno tikupanga ma rands iwo akupanga k2000 imodzi.. ndipo ife tikugwilizana nazo zoti dziko la malawi lilibe ndalama zotumizira anthu amene ali ku lendela coz akakugwila ukungokhalako 2months ndikukutulusa uyambenso kudya ma rands. pamene kale umakwela ndege wautali! mwachidule kuti mumve bwino ku jonz kulibe depoti kwa a malawi

    5. U are ryt bru lindela iz nt prison i waz dere b4 u feel free n eat chicken papa as well as rice komanso u have right to buy air ticket if u got money lke me i waz buyng air tick n go hom n nw i cam back bcz o can nt stay in malawi kumenekuja ndi kumochale baba

    6. Tsono mukamati smungakhale ku Malawi kamba koti ndi Mochale mukutanthauzanji? Kusonyeza kt makolo anu ndnso azibale anu onse akukhala ku Mochale? Kod ku Mochale mesa kumakhala anthu okufa? Tikamalemba tiziganiza kaye ndife a Malawi ndipo tikuyenera kulinyadila dziko lathu coz ndkomwe tinabadwira so tizamanyoze pomwe azibale athu ali konko

    7. Pls make money osamaiwala ka investment kuno kwanu, mwina kuudzabwera ukudwala umazapeza polilira. Just continue working hard osamaiwala abale kumawatumizila kangachepe. All the best.

    8. kumakhala kuvutika kubwera kuno,tinalowa mkalasi koma ntchito akunena kuti kulibe ndetikaba akumakatipha tikanena chilungamo pa iwo amene amakhudzidwa pankhani za cash gate(you the one call you mr #president

    9. mobisala bisala momwemo ndi mmene mulungu adandiyankhira ndikusangalala ine kuno pamalawi ndazuzika kufika pomakalimitsa mbale ya mgaiwa ufa kutha koma ndime yasatha ,pa jozi yehova kundidalitsa kupeza ntchito yabwino kupezaso banjaso labwino zomwe zimandisowa pa moyo wanga

    10. Kwanu nkwanu mthengo mudalaka njoka,enanu apa musayambe kutukwana kwanu.Mukayenda mudzisiya phazi cfkwa mulomowo udzakutsatani,abale anu mudasiya kumudziko musawaponye miyala.

    11. Anthu enanu mukungoyankhulapo chifukwa chotengera anzanu koma kuti tikuoneni or njinga mulibe koma matama basi…kumaganiza poyankhula…mwina ndi mau olilira mumafuna mutapita ku joni koma poyambila mulibe….ndiye samalani mmayankhulidwe mulungu adzakukanthani

    12. Kulira nditima palibe amene samafuna kuyenda tisanamizanepo apa koma zangokuvuta iwe amene sunasuthepo iwe khala koko uzigwila ukayidi wapanja chocho azako akuchita bwino ulira sunati ndindalama yako yikutulukayo unya nawo

    13. Anniettie Gobede chikwiri sometimes u better mind your own business they are not only Malawians suffering at Lindela en what u shld no ndalama yothandidzira anthu kuti azibwelera kwao pamene apedzeka mayiko a eni ndi ya United nation.Ngati ndinu ochita bwino kwanu u better continue asking God azipitiridza madalitso pa inu.Do want to tell me kuti kumudziko palibe ena akuvutika nkumathandidzidwa ndi boma???.Nanga those pple alibe manja.Note that Mulungu amapasa komanso amalanda so if u are blessed Madam Gobede Chikwiri say thanks to God simple osamatha mau anthu sakupempha chithandidzi I know in 3 month time they will be realised azikafufuza ntchito kapena kubwelera ku zintchito zao.Amapasa amalanda

    14. Henry u r right,we r here for better living so,amene muli ochita bwino Ku malawiko thokozani mulungu,nafe tikusaka mtendere kuno

    15. Henly Nkoko ukukamba zoona zokhazokha ndipo mfundo zako zili bho…. Mulungu ndi amene akutiteteza ife kuno ndipo yemweyo atetezanso omwe ali kulinderawo.

    16. OK. Do you imply that the government should not provide any means to take you back to Malawi? If you are happy at the waiting station then keep on staying.

    17. Osamalakhula ngati mwadya kalongonda,kukhala ku lindera bola kusiyana ndi ku malawi dziko losauka atsogoleri mbala zokhazokha ,ku yambira nyakwawa mpaka peter,ndiponso anthu ali kunja ndianzeru .anthu akamathawa mdziko Ndekuti utsogoleri kulephera,kwasara ndikuligulisa kwa trump

    18. Sitingafanane kumene chifukwa inuyo ndi opusa ndip nfana wa jonz sanama paliponse
      tapitan kumangoch mukaone u will tel me carz nyc houses are every whre

    19. Its tru… Ulindintendere sungayende kumakhala kuyesayesa kuti mwina, mkusunthika. I think umbuli ndiomwe umapangitsa. Coz kuyenda munthu umaphunzilanso zambiri. So Amalawi enawa umakhala umbuli chabe, amaiwala kuti mwai wawina nditsoka lawina. En palibe ofuna kukhala osauka padziko lino. Mulungu amapeleka mosiyanasiyana, coz anthu akulemela mkulimbika ntchito, kulikonse dziko lapansi. Sokeep your respect pls guys.

    20. kukhoma myumba za a galu,kudzala kapinga,ndixinazotero muziti greener pasture come back home. the guy you left him as a cleaner uja now he owns a cleaning service company & cleaning a lot of offices in town and he is doing good….it’s not where you work but ur business skills pipo….stop thinking kuti coz your staying ku joni illegally then u better than us. work up joni pipo

  135. Nkhanza chabe,boma likuiwala kuti anthu amenewa akuthandiza kutukula Malawi ndikangachepe komwe amapeza.Monga kuthandiza achibale awo powamangila nyumba,kuwagulila chakudya,kulipilila ana school fees ndi zina zambiri.
    Boma likuyenela kuchitapo kathu posatengela malamulo kuti akuti chani.
    Anthu amenewa akadakhala kuti adakali ku MW umbava kapena uhule ukadakula chifukwa chakusowa pogwira.
    Boma likuyenela kuifela lipeze ndalama zoti anthuwa abwele kuno sikuti azakhalatu abwelelanso ku SA kkkkkkkkkkkkkk pa anthu 100 mwina amene angasale ndi 4.I rest my case.

    1. Bro kachipande, i knw that but sizikusiyana ndi ndende bro coz mumakhala mkati basi,chimodzimodzi house arrested kkkkkkkkk

  136. I think boma linayesetsa pakatipa uku nkutopa tsaanu,, eeish! kkkkk zimati ena likuwasamutsa ali mma bus ena kuno akunyamukaso, komano vuto ndiloti Malawi wafika pamoto ootcha ndi mmatumbo momwe, sizikuyenda, anthu kukana kuba ndipake akumadzadzana kumeneku, kuno kwachuluka azitsogoleli adyela, ukati usolole zalaso anthu akungokuwamba ka brai basi, dziko lafika powawa ili

    1. Kkkkk Kom Mayamiko Nena Amvetsetse ANkhutukutu Amenewa Ndi2 & Ndizosasangalatsa Abale A2 Kumazuzika Choncho Chifukwa Chomwe Akupitira Kumeneko Ndikufuna Kupeza Zosowa Zapamoyo Wawo Watsiku Ndi Tsiku.

    2. Munthu akhala bwanji kuno yet maganyu akuvuta, pamene ukoko pang’ono pokha akutha kumasiyanitsabe ndikukhala kuno, zimangovuta ikafika situation ngati iyiyi koma kwathu kuno life yafikapo especially kwa munthu oti akungokhala, awa amalemba zosimbwawa nkuti iwowa ali mzintchito zabwino monthly akulandila ndiye osamawadabwa

    3. Kmanso choti mudziwe sionse amaene amapita ku joni,anali mmavuto kumudxi kuno chimakhala chisankho kt ndikakhale ku joni pamene kuno atachita kusiya zopanga zawo zomwe zimawayenderanso kwambiri,ndiye kwaanthu amene amavutikawo kuno mzoonadi malawi wakwiya kma nanga titani zavuta zatha

  137. tinabwela tokha ndipo zotionekela zimationekela tokha…Mulungu nde alinjira zothandizila bola moyo kwathuko tizafika afuneasafune.zachamba munatipasa yobwelela kuno…siyani sitingakulileni.ndalama zomwe mumapeleka kuzatengela anthu ndimusonkho wathu womwe tinapeleka tili kumeneko komaso pobwela kuno….komaso abale athu ndamene amapeleka zimenezo.sizambwiyanu.mwandikwana anthu opussa inu.

  138. Kodi kale lonse zimakhala bwanji? nde inuyo tsopano ndiamene mukuziwa Malamulo kwambiri? Khani zina mukamanena or kulakhulapo muziganiza Kaye B4, oky Lero dziku lathu likuvuti ndi njala inuyo mutipo bwanji pamenepo? Zinazi zimangooneseratu kuti izi ndi mbuzi zophuzira zolemera zanyera. Now ngat kuli kuba beranituni, kupha pheranitu, kunama namiranitu, idzakwana thawi yotifuna pano Amalawi tinachenjera muzaziwaso! Mukumati aliyense amene watuluka dziko lino tamuchosa mkaundola wadziko lino hahhahah zitsilu zolemela

Comments are closed.