Zivuta ku Sunagogi pamene Mai Clinton aluza zisankho

Advertisement
TB Joshua SCOAN

Zisankho za mu dziko la Amereka zasokoneza utumiki wa mkulu wa ku Nigeria otchuka ndi nkhani za ulosi, a TB Joshua.

Lachiwili pa 8 November anthu anavotela Bambo Donald Trump kuti ndiye akhale mtsogoleri wa dziko la Amereka akachoka a Barack Obama chaka chamawa.

TB Joshual Hillary Clinton Donald Trump US Elections Nigeria
Zamuvuta Joshua

Kupambana kwa Bambo Trump kwasokoneza mitu anthu ambiri amene amayesa kuti a Mayi Hillary Clinton apambana. Mayi Clinton amene anakhalapo ndi udindo mu ulamulilo wa a Obama amaoneka a chikoka ndi okondedwa.

Chikoka chawo chinasokoneza mutu mtumiki wa Mulungu TB Joshua mpaka anapanga ulosi oti Mayi Clinton apambana.

“Ambuye wandionetsela za zisankho za mu dziko la Amereka,” anatelo Bambo Joshua amene ananenelapo za imfa ya mtsogoleri wa kale wa dziko lino a Bingu wa Mutharika.

“Ine ndikuuzeni kuti Ambuye akuti apambane ndi mzimayi,” Bambo Joshua ananetelo uku owatsatila akutchaya ma Ameni.

Koma zotsatila za zisankho zitatuluka, a Joshua anapezeka kuti ananama.

“Wawina zisankho ndi munthu wammuna, iwo aja bwanji amati azakhala wamkazi?” anafunsa choncho anthu odabwa.

Advertisement

392 Comments

  1. Moses ndi Mirriam akanakuletsani izi. Bola mirriam anapanga khate koma mwina chilango cha onyoza chikhala temberero which lasts for 4 generations.

  2. nonse amene mumakhulupilila. maprophets mumakhala ngati mulibe nzimu mumayendela ziwanda osati mulungu kapena satana onyenga ngati maprophets

  3. Jeremiah 14vs14..When a prophet speaketh in the name of the LORD, if the thing follow not, nor come to pass, that is the thing which the LORD hath not spoken, but the prophet hath spoken it presumptuously: thou shalt not be afraid of him

  4. Kaya ine zaulosi ndili nazo kutali coz kwathuku kuchislam kulibe nyasi zaulosi timamvera kwainu amzathu ndiye mulungu wafuna kudzachitisa manyaxi ma so called prophets

  5. mulungu simunthu. ndipo ngakhale atafuna kuti inu Lero mutchulidwe dzina loti maliro zimatheka. nde uyo mukumunenayo mmmmmmmm ayi amangolosera koma wokwanilitsa ndi yehova basi.

  6. Zovuta izii pray hard, read the bible bola asakhale mzake wa bushiri chifukwa bushri ndiye ndiwasatanic kma mkulu uyuyu mwna zangovuta ine itrust hm 90% bushiri 0%….zofunikira osalimbana ndi anthu prophets, pastors etc its waste of tm rather focus on ur relationshp wt God!!! Is it gd or nt,, the holy sprlt wl direct u n everythng!!

  7. if GOD wrote he wrote stop bleme one anether bcz only God knows the trueth, jesus says if some preaching the word of GOD in the name father, son & holy sprit, he is son of GOD leave TB JOSHUA to preach the word of GOD, just repeat ur sins and follow jesus ways to have life, GOD say s , otembereledwa ose onyoza mtumiki awamulungu.

  8. Inu a news a ku Malawi please please muzimva chinzungu amanenera kuti please tell if you was there last Sunday mene amanena bwinotu

  9. PVT: God and his Prophect they are never wrong on American election ,actually the popular vote . Hillary Clinton she win Trump as 47.7% to 47.5%. She got 59,755,284 votes , Trump got 59,535,522 votes ,actually Hillary Colinton she narrow win 0.2% as Prophet T B Joshua told us at the Sunday Service . in God’s opinion She is the winner of this election ,but we human being’s system maybe against God’s will …
    Glory be to God ,thank you Lord, thank you Prophect T B Joshua …

    1. Mutale Nsomeka, if you really understood the electoral process of the USA (especially that of the president), you couldn’t have been scribbling this gibberish. However, I take it that u are a “Prophet” fan, and I understand that. But if I were you, I couldn’t have been wasting my time defending the indefensible. TB Joshua goofed (and for your own enlightenment, he has erased the tweet that proclaimed what you are unconsciously denying). That is it. And please stop this nonsense of “God’s opinions”; you make God look stupid (a thing that He is not and cannot be). God never has opinions; Hillary lost. And if you are really a Christian you would want to read Romans 13:1.

  10. He he he he ndiye zakhalilamu Mr joshua akut chanino,tiuzeni anthunu amene mumansatilanu.apa drivelayu wakulowesani tchile ndiye mutani muzinkhulupilirabe kaya

  11. TB joshual wanama kokwana phanvu zake nzochokera kumidima mumadziwana kunyanja komko koma choti mudziwe akuluakulu mulungu akamuongola muthu palibe omusocheresa chimodzimodziso amene walandila mkwiyo wamulungu palibe omuongola nde ine sindimadabwa muthu akamakakamila tchimo olo ataona kuti chilungamo ndi ichi satembenuka muzichedwa mkumakonda athu oti ndasasatana onamizila yesu chisomo sichinakugwereni utumiki wamulungu sumangobwera ngat phepo ayi atumiki enienu amulungu adapita kale panopa anatsala mautumiki onyenga mmalo mowauza athu azilapa mukukangalika kuwapatsa athu zamdziko zomwe zisakhalitsa zoti kulichilango chamulungu mudayiwala TB Josual ndi ena omwe amazitcha ndatumiki amulungu asaliodzidzedwa ndimulungu mudziwe mulindimilandu tsiku kachiweruzo mukusocheretsa mitundu ya athu ndipo nmukayakha komaso chilango chowawitsa chikukudikililani moto waukali ulipansana panu musiye kumawanamiza athu athu ambili piano akungofuna zadziko lapasi ambili mudzawaone amapita chifukwa chamatenda kusowa kwabanja ndi mavuto ambili sapitika chipumutso chamukungu dziwani kuti ndithu kusauka sitchimo kupanda mwana sitchimo ayi lelo osauka amaoneka kuti adamulakwila mulungu ameneo amakhala mayesero amulungu musiye kuzitayitsa thawi ndikuyang’ana chipulumutso kwamuthu nzanu olengedwa TB Joshual is a DEVIL LIAR STOP MISREAD PEOPL MOTO UKUKUDIKILILANI

  12. I don’t trust a man,God will remain himself and he cannot be corrupted by the evil people’s mindsets .Prophets are just competing for their own popularity.

  13. Nawenso chisilu chamuthu ana kuuza zoti mulungu ali ndimwana ndani zachamba basi mulungu alibe mwana tazingokambani zina apa osati zoti mukalowe kumotozi pepherani kasanu pasiku mulungu akakuloweseni kumwamba

  14. Chitsanzo chabwino chimenechi musamakhulupilire anthu aziwanda. Anthu onama mdzina la Yesu. Akupanga zimene Yesu sanapangeko

  15. Hahahaha,,, ife kuma followers ake onse tingoti pepani, ndimmene zidzakhaliranso pa tsiku lomaliza, mudzakhumudwanso, msanati.hehehehehe! Ine pheee mwayesu

  16. anthu opusa ndi amene amamutenga TB joshua ngati amaziwa chili chonse ,inu mwini dziko lapansi ndi mulungu iye ndi amene amaziwa chomwe chingachite mawa osati munthu olongedwa .

  17. Vuto la atolankhani komanso ma prophet alero amakhulupirira kuti chipani cholamula sichiluza koma imeneyo ndi mbiri ya kale zakachitika madera ambiri ngakhale kuno ku africa including malawi 2014 dpp inagwetsa pp komabe onsewa adali m ‘boma kungoti dpp inali pa bench kwa 2yrs zikanakhalabwino ikanawina mcp?????????

  18. I thought we should preach about God’s kingdom, kodi zaumulungu nzogwilizananso ndi ndale? always prophesis about politics, osamvako zakumwamba why? guys, lets open our eyes and see….

  19. anthu timatengeka ndi zinthu zopanda pake. Ati uyu amapanga zozwizwa akandipemphelere mmmmm mumabvutkiranji? Lowani mu chipinda chanu Gwadani pansi pemphani kwa mulungu wanu azakupasani zosowa zanu. Masiku osiriza kuzaza aneneri onyenga azasamusa phiri kuchosa uku kupitisa uko anthu nkumati uyu ndi mwana wa mulungu uyu. Ai ndithu ndithu Tisapusisike. Nanga Taonani ulosi uwu . Zikugwirizana?? Ngatidi amalosera mu zowona nanga zatani? Mulungu salakwisa. Mwina uyu anaiwala? Tisatengeke ndi zinthu zopanda pake. Tizakhumudwa tizasiya kukhulupira mulungu Titakhumudwa ndi zochita za ma prophet

  20. KKKKK mukundiuza kuti nthawi yonseyi simumadziwa kuti Joshua ndiwabodza I don’t believe in these guys so called Prophets ena ndima drug dealers inu kumawatcha men of God kkkkkkkkk and why prophets are always Africans? Tell me!!!

  21. Kk pali mulotsi mmozi yekha ndiye mwana wamulungu amene tsanama.amene tikumu dikila kuti akati konzele malo bas zonamiza apa ay.

  22. Kikikikikikiki…..akuti he was just trying to predict whats gonna happen, it wasn’t a prophecy, kikikikikikikikikikikikikikiki zinakati zatheka anakati it was alrdy prophesised but coz zavuta akuti it was just a prediction, it wasn’t a prophency as you people thought…..kikikikikkikiki

    1. Victoria Mithi ndiwe wamisala or u were born prematurely.Wouma mutu ndipo sudzathekha !Pepa!

  23. who are you defending lies,@ he said we should pray against that,so which means he was saying people should pray that the woman shouldn’t win?

  24. Only this time God he used me to prophecy about this just look on my wall you will see what I mean God bless you people of God amen

  25. Ndikugwiridzana ndi frank chitule .abale ndi alongo choyamba ziwani kuti nthawi yomwe tili ino ino ili ngati extra time .yesu ananena kuti anthu adzakhala okonda ndrama aukali mtundu ndi mtundu udzaukirana.aneneri ambiri adzabwera mu dzina LA yesu.ndipo izi zikuchitika ndi nthawi yoti tilimbikire kupemphera komanso ma prophet onyengawa tiziwapempherera kuti adzapitiridze kusocheretsa anthu a yehova nthawi yatha

  26. Bas manyazi kwaotsatila joshua’nu anthu opanda mzimu Ana anjokainu bwanji chikhulupililochanu mumaoka kumunthu??

  27. Apa ndi pamene mungadziwe kuti prophet ndi wonama, wotsogozedwa ndi ziwanda komanso wa satanic ndiye ndi zanu izo nonse mumamvera oipa ameneyu

  28. Aneneri onyenga Yesu sanaloserepo za dziko ngati zimenezi! Lol .Kuli uchimo wambiri womwe ukuchitika padziko lapasi bwanji osalalikira za chipulumutso, koma ngani ingokhala kudalitsika ku dziko lapansi, you will be blessed! Successful messages only.

  29. Aneneri onyenga Yesu sanaloserepo za dziko ngati zimenezi! Lol .Kuli uchimo wambiri womwe ukuchitika padziko lapasi bwanji osalalikira za chipulumutso, koma ngani ingokhala kudalitsika ku dziko lapansi, you will be blessed! Successful messages only.

    1. Nanga zamtengo wamkuyu unanyala uja. Nanga za Jerusalemu ndi kachisi ndi mwala yake? Mauneneri onse a prophet T. B ndawaona akuchitika and ndimamukhulupirira Mr John Ngwenya

  30. Pali zinthu zina Mulungu amafina muone chilungamo koma mumachita kutseka maso ndimakhutu, chifukwa chilungocho chikukuwawani.

    Asaza pangeso predict koma azingo phunzisa zakubweranso kwaYESU, alarikile ndiku phunzisa za kuti anthu atembenuke mitima. Osatiso kuma khala akulimbana ndizadziko lapansi.

  31. Kkkkkk.. Donald Trump has won the electoral vote while the popular vote has gone to Hillary clinton…. according to US policy, electoral vote takes someone to the white House… wht ever the case.. Ibelieve Prophate TB Joshua 100%.. and ucant compare TB Joshua with Bushiri the childish fake prophate…

  32. Amalawi kupusa basi,osamalimbana ndi president wanuyi bwanji,mmalo molimbana ndi pitala kuti athetse mavuto a mudziko lanu but ur busy talking nonsense about the man of God, wat is ur benefit from this story while ur sleeping without food in ur house? kupusa basi,n some of u u even dnt anything about this man of God but busy talking shit.

  33. Zopanda ntchito izi Mulungu anatiuza kale aneneli ake mma holy books kuyambila bible mpaka Quran mulibe mayina awo

  34. heeeee! ndiye Mulungu ameneyo alibe chibale phwanga, amakwangwanula tima plan nditi nzeru tonse tamamina ta woyipayo ndikutiyika mmaja mwa tiyana ngati pamenepa kuti wuwonekere. Ndie ana amagwiradi nawe tchito kukumoka ngati mmene akubebera ma comment wukawa browser nkumati koma nzedi. take care ndi boma lina kumwamba and I think wakhalaso winayu iweso usamale ndi boma limeneli lakumwamba. YEHOVA ndie mwini ma plan ubweraso poyera naweso ngat nzakoyu. wekha osati ife. Ndiye poti ndiwe kaleso m’bale ayi mmwemo ine ndidzango kukhululukira koma sindikudziwako ena kuti adzakutani.

  35. heeeee! ndiye Mulungu amene alibe chibale, amakwangwanula tima plan nditinzeru ta woyipayo ndkutiyika mmaja mwa tiyana kuti wuwonekere. takje care and I think wakhalaso winayu iweso usamale ndi boma lakumwamba. YEHOVA ndie mwini ma plan ubweraso poyera nawe ngat nzakoyu. wekha osati ife.

  36. Ana a Njoka amamutchula kuti ”Man of god” Kupepela basi!!!! Koma nkumazitcha kuti ndi Achrisitu pamene BIBLE simulidziwa.what a Shame!!

  37. Amalawi muzitengebwino mumawonjeza ndizotengekatengeka apondiye mwaziwonelanokha mwanunokha mulisoutumiki komamumazikayikila mumagosatila zilizose mulungu alipalipose matumiki enawa samalani amalawa musapusike ndkutchuka amalawi mulungu amakukondani ( ambuye pitilizani kudalisa malawi ameee )

  38. Munthu yemwe amamukhulupilira TB Joshua nd otaika kodi iyeyu ngat amaona zatsogolo nanga bwanji sanalotsele zoti church yake izagwa pa chifukwa chan? Uyu nd wapansi pa madzi

  39. mistake. Bible limaletsa kunyoza azitumiki ake sindikumubakira Joshua koma yense wakunyoza ntumiki wamulungu azalangidwa. simukudziwa chilungamo yet mukunyoza apa kupalamura gahena ya moto ndithu. yense amene akutumikira dzina lamulungu wether nd ntumiki wabodza or ndiwowona musanyoze. who r we to judge? abale ndi alongo samalani Mulungu azalanga ekha zikomo kumpando

    1. Linatitu kunyoza ntumiki wamulungu linapatuliratu kut alikonso ena satumiki amulungu.Alimbanabwanji ndi za ndale ngat kut zugwilizana ndi umulungu?

  40. Ma prophet Enawa Amandidabwisa Avekele Mwezi Uno Miracle Mabanja Kaya Ku tchito. Miracle ikachitikad Aziti Ndye Walosela!Kumatenga Petrol Mkumasakaniza kaya Ndizichani Mkumati Anointing Oil Ati kumazisila Pamutu Pawo cholinga inu Poona Muli Ndiziyenda Ndimadaliso.Ayi Ma prophet Osewa Ali pa Busnes Bwanji samanena Za ufumu Wakumwamba?Amangolimbikila Muzapeza Banja,Ntchito,Busnes koma Amaiwala Zaufumu Uli Mwamba Kuutchula.Chongofunika Anthu Ngati Awa akungofuna Chuma chanu Basi. Wakuva Wava! Osava Kaya Atsate Uzatiuza!

  41. Khalani kumaweruza azanu mulungu ndi amene adzawereze inu stana anayamba ndikale kulimbana ndi TBJ Koma ndikuwuzeni ichi satana alinanu cholinga mukapanda kusamala mumutsatadi

  42. Thanani ndimavuto anu kaye.Dziko lingosaukirabe,magetsi tidayiwala,njala ndiimeneyi,pano tafika pozolowera kuunikira makandulo nde muli busy kulimbana ndi TBJ mmalo molimbana ndiakukuberani ndalamawa.

  43. Atumiki amasuku ano ambiri siatumiki amulungu koma ongokamba zofuna zathupi chonde tiyenera kuwapewa chifukwa akutikopa kudzera mudzina la mulungu. Zolosera zawo zazii zongofuna kudanitsa anthu. Always believe in God not a person!

  44. abale tiyeni tizingolimbikila kupemphela TB J ndi munthu obadwa muthupi lanyama tiyeni tisamukhulupilile.GOD Z GD O THE TYM!

  45. chonde guyz zomanyoza atumik sizabwino kwa amene timamukonda TB joshua tien tipitilizebe kumukonda chfkw amene akumunyozawa amadana naye ndikale nde asatipangise kut tizinyoza atumik kut muone amene akudana nd tb joshua nd anthu ot sapephera ndkomwe azizanga tisatengere azizathuwa zikomo powerenga

  46. Utumiki wausatana uja, mzake nd uyu wathuwathu akhala kujon yu, mukamapita kwaana anjoka amenewa skut mukapemphera koma mukatenga zwanda. Zopusaaaa….

    1. Frankly spearking Mr Elia, if TB Joshua had that prophecy then it means that that Prophecy wasn’t from God, because God can’t reveal lies to His Messangers. Its not a fight, people are talking what they heared from TB J, so they need an explaination about that Prophecy!

  47. Don’t hesitate we’re in the last days now all the holy scriptures must revealed Jesus himself prophesied about these days Matthew 24:1…..

  48. TimakuuZani ife kuti PROPHET silimabwela kwamunthu yemwe wakhuta kondoole kungoloweza ma ves awiri basi uprophet umabwera pokumana ndi mgero live sati zanuzo musazakhulupilireso

  49. Hahahahahah guys why can’t we concentrate with our own country on how we can remove poverty in our country….. We are just talking about american president as if we will gain something at the end… Grow people of malawi shaaaaaaaaa

  50. Koma asamaname ngati mene amanamidzila anthu mu church lake lija kumawagudubusa anthu ndi masenga ake aja ife ai sitimakhulupilira munthu timakhulupilira modzi ndye yesu khristu basi osati izi

  51. TB Joshua timing inamuvuta akanangotengera mene zisankho zinaendera kumalawi pano bwezi anthu akumutengabe dolo nkumawapusisabe koma apa yalakwa

  52. We are in the last days as prophesied by Jesus Christ,many will come in God’s name,wearing the name ” lamb” but they are wolves or heyanas

  53. A prophet is a human being not all prophecy can come from God coz he is human whether u like or not TB Joshua is a man of God in addition l don’t believe he prophesied like that if he did let us believe is human being but believe that is a great prophet in the world

  54. Khulupirirani Mulungu osati munthu chifukwa munthu amakhumudwitsa! Mulungu atayang’ana kudziko la pansi, anaona kuti palibe ndi mmodzi yemwe ali olungama. Kotero tonse ndife operewera ndithu pa ulemerero wake. Pamenepa sanasankhe kuti uyu ndi mneneri kapena ayi. Ndiye tikhulupilira bwanji munthu pamenepa? Chipulumutso sichidzaona chuma kapena kutchuka kwa munthu, mchifukwa chiyani azineneri ambiri ziphunzitso zao zimasamira pa chuma? Ambiri apa akhumudwa ndi ulosiwu kuiwala kuti iyeso ndi munthu ndipo ali ndi zofooka zakeso pa Mulungu.

    1. Plz tikamawerenga bible,choyamba tikuyenera kupempha Mzimu Oyera kuti atitsogolere. Kupanda kutero titha kuwerenga koma osatolapo kanthu. Kodi mchifukwa chiyani Yesu za ufumu wa kumwamba adayerekezera pa tiana tating’ono? Kodi mchifukwa ninji Mzimu Oyera umaonekera ku anthu kudzera mu mbalame yotchedwa nkhunda? Kodi mukawerenga nkhani ya Lazaro waumphawi ndi Wachuma uja zimatiphumzitsa chiyani? Taonani Hanania ndi Safila adalonjeza Mulungu pa chuma chao mpaka kugulitsa munda koma chisoni sanapereke chonse mpaka awiriwo anafa. Kuti tipeze chipulumutso tikuyenera kudzichepetsa monga tiana,kukhala ofatsa mtima monga nkhunda. Munthu amakhala waulemu,ozichepetsa komaso kudziwa Mulungu pomwe ali osauka koma kungopeza chuma zonsezi amaiwala mkuyamba kuzikweza,kuzitamandira etc. Zotsatira zake timasemphana ndi Mulungu mchifukwa chake panabwera mau oti ndi kovuta munthu wachuma kukalowa mu ufumu wa Mulungu. Naneso ndine yani pamaso pake? AMEN!!

  55. Tembenukani ndipo mukhalenawo moyo osatha Landilani Yesu mumtimamwanu lolani machitachitaanu afanane ndi a Yesu mwana wa Mulungu! Kuuzimu kuli zochitika zambiri koma Zitengera kumvetsetsa ndikudzipeleka kwa wakufunakuzimva! Ndani amene adzapezeke dzaka 60 dzikubwelazi? Tifune tisafune kudzakhala tonse amene tikuwelenga uthengawu tilipansipanthaka kudukira chiweluzo ngati tingachitike mwayi mkatimwandimemomwemu Yesu akhonza kubwera kudzatenga(oyera mtima) mwai ukadalipo koma siokakamiza

    1. Mmmm!This is powerful,,,thanks for the word,iam realy touched togather with my soul amen and amen,God bless u my brother

  56. Anthu mumamalephera kumvesesa sananene mukuneneramo plz kkk paja mumayang’ana zolakwika osati zolondola god must forgive the admin of this page

  57. We shudnt be worried about TB Joshua unfulfilled prophesy here. Donald Trump has won, congratulations to him and Americans for their wise choice. As for us malawians we are still stuck with our peter mutharika who is slowly but sure driving us to the grave. I hope DT will help africans drive out these corrupt leaders like peter mutharika.

    1. Nkhani zake nzogwirana, Trump ananena kuti akazawina azathana ndi azitsogoleri obera anthu aku africa. He has won and hopefully athana ndi anthu ngati achina pitala oonelera katangale. Munthu akamabisa anthu akuba ndekuti iyenso ndi mbava.

    2. Pitala yamukhuza bcoz he is a corrupt leader, Trump will deal with these corrupt leaders. Prophesy kwa ife ilibe nctchito chifukwa analosera ndi prophet waku nigeria, zisankho zaku America. Ife vuto lathu ndi pitala amene akuteteza mbava za cashgate bcoz iyenso ndi cashgater.

    3. Kkkk once u write something about peter mutharika u attract lots of attention and replies. Koma ndipemphe nao kwa inu ondinyoza. I did not ask for ur opinion on this comment. Keep ur rath to urself.

    4. Those who talk about just show how they fear him. There is no way trump can deal with other leaders. That’s a total lie. Akulephera a ICC. Iye ndye ndan

    5. Trump promised regime changes of some countries in africa, i hope he will do just that in Countries like zim, uganda. Azatithandizeso ku malawi we lack gud leadership.

  58. Kodi mulungu wayamba kumunamiza? He must only do Godly job not including politics. Theres nothing like that to the creater

    1. May God forgive you, you don’t the power to jugde, that belongs to God alone. You have been cursed the solution is repentance. Ur blind and you don’t even see or here what is in the spirit. Devil is behind your back

    1. Chiwaya. …
      My God has forgiven Josua for his misleading prophecy….Mulungu sanama….sono wa josua uyu akunama bwanji

  59. Amalawi kodi tinakhala bwanji ? Basi paliponse kufuna kulakwitsa . Mumvetseleso ndiye mumve kuti anati chani . Ngati mukufuna popangila ndalama Koma ndiye zakukanikani chifukwa mwini wake wakumwamba akuwonani ndiye tsiku lina mudzayaluka ndibodza lanulo.

  60. Wati uilembe mchichewatu cholinga anthu anyoze utumiki wa joshua mokukomera? Shame on u! Besides, palibe chavuta ku sunagoge

  61. Munthu ngati analephera kulosera zakugwa kwa church yake nde akalosere za chisankho.ndipo amalawi nchifukwa umphawi sumatichoka kupepera too much.mmene zilili apa munthu nkumabakila joshua??? ¡aaaaaa zakuntoso basi

    1. Tikamati analephela kulosela zake zomwe, tizikumbukaso kuti, nthawi ya Yesu ena anamuuzaso Yesu kuti adzipulumutse yekha ngati ali mwana wa mesiya koma sanatelo. Zinthu zina amadziwa yekha Mulungu ndizolinga zake.

    2. That doesn’t make him a false prophet!, Tb Joshua is an anointed servant of God.Don’t play with men of God otherwise you’ll kindle God’s wrath upon thy very self. However, Jesus Christ loves u & HE wants to save your soul. God bless u!

    3. I will always like pastor Chris he always emphasise that everyone is an anointed as long as he/she has Christ Jesus he/she can do everything through Christ who gives strength…You are a prophet of your life————————–

    4. Kaya sikundikhuza poti kwathuku kuchislam kulibe nyasizi mumat zaulosi timamvera kwainu koma munthu wanzeru sangaganize munthu akulephera kulosera zake zomwe ndiye akalosere zaena.kumaganiza pena pake

  62. fake man of God.nde ena inu mudagundika like page lake ngat akupasani ma RAND KAPENA MA METICAL KAPENA MAKWACHA,apa mbiri zaulosi zamvuta and people will never trust him,adalosera zot by october to april malawi and zimbabwe will lose apm,so mene apm wathu amadwala timati mwina josua walotadi,ooo mulungu wanga,apm adati “no any person will cause his death.”and pa malawi 24 this story posted and mudamunyoza kwambiri apm kumati iye ndindani pamaso pa mulungu,ngat atumiki alosera that mean its from god,padali foto ya josua,bushir and wina wake nkhwangwala osaziwika bwino,lero president ali moyo,dzanja la mulungu lamukakha kt ayi mwana wanga bwerera,awo ndi asatana a josua and bushir,zamanyazi.so today same same fake story kkkk zachamba.

  63. Ndikanakhala TB JOSHUA ndikananena kuti sumunave mbwino ndinati a wine ndi mzibambo osati mzimai, kutheka anthu anachita haki account yanga ndikusintha.

  64. Am not like to heal someone saying that #joshau is man of God,kodi iweyo ukunena iwe simuthu wamulungu?who are u,if u are not belong to god and where are u coming from.munthu wazelu angapite kwamuthu kuti amupephelele iye samaziwa kupephela kupusa kwa African kkkkkkkkk

  65. Nde tikamati sibwino kukhulupilira ma #Prophet wa coz sionse omwe ali owona,lero ndiziti,,,,,ndizimenezi nthawi ikukwana yoti ma #Prophet onyenga ayaluke

  66. apa wachita bho kuyikadi chichewa…kkkk ameneyo wagwa nayo ndipo ma bp ashuta..alibusy anthu kumuyikila kumbuyo…yesu pamateyu24v24 ananena kale zaneneri onyengawa..pano olo nkhope ikuonesa kuti njamatenga Achikulile aYoswawo.mwina DJ wawinayo ndishemale pano.omwe mukumuyikila lumbuyo munali kuti pazana akulosela kukana kuti sananene..lelo zakuvutani.

  67. Iwe joshua!! Ndi azilongo akowo…ndati ndikuuzen kut zomwe munachita 2012 chaka chino mulephera. ..kodi iyeyo Joshua ngt amaona zakusogolo analora bwanj tchalitchi chake kugwa anthu 90 mkumwalira….bwanj sanaziimise zimenezo? Kusonyeza kut munthu uja ndi wabodza kkklkk #hashtag_ndinamva_kanyamakaz_pang’ono

  68. Ineyo sindimawamvetsetsa a Malawi ena amene amawatenga ma prophet ngati Mulungu komatu Bible limanena momveka bwino kuti masiku otsiriza kudzauka aneneri onyenga… Tiyeni tigalamuke

  69. Komatu iyeyo salalakwitse zimach itika ndithu muthu kulosela koma zithu osachitika ndiye musaone ngati zachiledo apapa komaso ma vote sanaponyedwe ineso ndili mbali ya TB joushe yemweyo sananame ayi clenton awina ndithu

    1. Prophesy ya Mulungu salakwitsa & Mulungu salakwitsa.Zaonekelatu kut prophesy imenei siyochokela kwa Mulungu,munthu ndamene amalakwitsa nde a prophet anuwa alakwitsa coz mphamvu zopangila prophesy yawo sizichoka kwa Mulungu.

    2. Chiti muziwe ndi ichi munthu umalakwitsa kumene iyeyu sikuti amanama ayi koma pali zithu zina zomwe zikumuyenda pa nthupi lake ndithu ndipo tiyeni tinkhale tiziona zomwe zichitike kapena kuziva kuti ku America kwachitika zakuti muonaso

    3. Thanx mwavomela kut iyeyu amapanga ma prophesy ake mu umunthu osati mu uMulungu,nde ma prophesy aumunthu its blasphemy.Pitani mu Bible lanu,simungakapeze zoti prophesy ya Mulungu inakanika.Mutaya chipulumutso pokhulupila mneneri onyengayu mmalo mokhulupira Yesu khristu mamuna wa mtanda.

  70. eeeee people mumanva chizungu kma???????? he said ‘i c a woman becoming the president of america,we should pray against that” nde wea a u getting that info yot amat clinton awina??? vetseranson prophecy ija!!!

    1. mudwaladi koopsa kkkk kodi iwe akamati woman analiko angati mawoman ku zisankho zaku amerika omwe anayimila???inu ndembuli wachizungu..muneneri waboza Yoswa mateyu24vs24 wagwa nayo…kodi ngati u prayed for that bwanji mapemphero anu athela munjila osakwanilisidwa…ngwabodza..ma bp akwela kumeneko mwakhaula.

    2. zopusa eti TB Joshua’yo mukukhala ngat agogo anu bwnji…ur backn em as if anakupatsaniko ya cupon bwanji??? eeeeeh kume amat Clinton awina.! hihihi nde bolaso mukana backila bushiri asopan Rather TB..chifukwa bushiri mukhoza kupemphako madzi akumwa kwawo cz ndiwakonkuno evn naeso mabodza too mch

    3. TB adanena straight and kutsindika pa fb page yake kuti i see woman winning in US election with narrow gap.And status waifutapo,panalibe mawu oti we have to pray njeee and if you still doubting i can send you his status.

    4. iwe ndiwabodza ndithu. ukuona ngat sitinawelenge ife? mbuz yanuyo mukapsa nayo. inaleka bwanji kulosela zakugwa kwa tchalitchi chake chija

    5. Mbatama imenei I think ndiyakumidimaso pagulu osamaoneka ngati ozimdikila kwambili umazakhalaso chisiru chenicheni sindimafuna kuperekako maganizo koma zandikhudza kwambili masiku omaliza muzaona izi. …

    6. #Mphatso on fb was to inform other ppo who couldn’t afford to watch him on TV and it is him who wrote that massage on Facebook thats why he have deleted it.And it is not first time for him to tell ppo lies.He prophesied last month about Nyovest that ppo will die at Orlando stadium but nothing happened, why you backing him? the whole world knows that he have lied about election and this news is everywhere now.

    7. Inu tisakangane ndizoona TP JOSHUA ndiwabodzaa, nanga bwanji amangochotsa utengawo umene anatumiza pafb???azipanga za Mulungu zinazo zasatanic kkkkkkk

    8. It doesn’t matter how much you will try to back your con man, he lied and goofed big-time and there is nothing you can do about it! He never said anything about praying against it. The clip has just proved to you that you are liars trying to justify a lie. Hahaha zavuta ku SCOAN!! Sorry blind followers!

    9. Wamkonda chabe mtumiki wakoyo, ife tingoti pepa wakukhumudwitsa, tsiku lomaliza adzakukhumudwitsanso chimodzimozi . hehehehe! Uluuuu

    10. no matter what pple say against the man of Gid but note that, this cnt change him so dont waste your time saying bad things about him kuopakuutsa mkwiyo wa Mulungu.

    11. Watch out prophecy has no time flame. You can dance today and weep tomorrow. The holy spirit does not lie. One day a woman shall take charge of USA. Dont blame this man of God.

    12. #wellington nowa there will be a woman president as well as Chinese president a Latino president any one can be a president to claim to prophecise that is dumbness.

  71. Mulungu sana kuteleko mulungu amangofuna kuwaphunzisa akuluwa kuti palibe amene amadziwa za mawa. Tsibwino kutengeka ndi anthu ngati awa mudzakhudwa koma Mulungu sakhumudwisa.

  72. NDIYE CHANI AMATI TB JOSHUA NDI MULUNGU NDANI MWASOWA ZOLEMBA ETI KAGWERENI UKO OSAMALIMBANA NDI ATHU A MULUNGU ALIYENSE MUMALIMBANA NAYE OLO ATABWERASO YESU KHRISTU MUZALIMBANA NAYESO GO TO HELLL NDI NKHANI YAKO YOPANDA MUTUYI

Comments are closed.