A Malawi apemphedwa kuti azilola amayi kuchotsa mimba

Advertisement

A Malawi apemphedwa kuti akhale anthu omvetsetsa pa nkhani ya lamulo lokhudzana ndi kuchotsa mimba.

Malamulo ololeza kuchotsa pakati akufunika ku Malawi.
Malamulo ololeza kuchotsa pakati akufunika ku Malawi.

Malingana ndi mkulu wa bungwe loona kuti palibe kusiyana pakati pa akazi ndi amuna, la Gender Coordination Network, Mayi Emma Kaliya, a Malawi akuyenela kukhala anthu olola kuti lamulo limeneli liikidwe.

Pakhala pali mpungwepungwe pakati pa a Malawi pamene ena akufuna kuti amayi aziloledwa kuchotsa mimba koma ena, maka atsogoleri a mipingo akukana kuti ayi. Iwo ati chifukwa kuchotsa mimba ndi kupha.

Koma onse ogwilizana ndi kulola kuti amayi azichotsa mimba ati dziko silingamalamulidwe ndi malamulo a Chalichi. Enanso akuti mchitidwe ochotsa mimba umachitika ndi kale koma mwa njira zosayenelela.

“A Malawi akuyenela kugwilizana ndi lamulo lovomela kuchotsa mimba ili kuti titeze amayi ndi asungwana amene akufa Kamba kochotsa pakati,” anatelo a Kaliya.

A Phungu a kunyumba ya malamulo akuyembekezeka kukambilana za nkhaniyi.

 

Advertisement

246 Comments

  1. Dziko la satanali latsaladi pang’ono kuwonengedwa,dzowonadi amalawi kuvomeleza muchitidwe woyipawu? Izi ndizomwe ananena yesu kut mumatsiku womaliza muzawona ndi kumva zinthu zowopya.

  2. I mean that’s foolish thing coz simukuganiza et bwanji zotere zikabwera musanabadwe bwez mulipo imu enanutu mukuyakhula zopusa enanutu munabadwira kuchigololo chif

  3. A Malawi ake atiwo munena inuwo ?,zopusa eti za usatana ife ayi.makondomu ntchito yake ndi chani ?,kungozolowera kupha basi ifeyo makolo athu akanaganiza zopusazo kapena inuyo makolo anu bwenzi muli pamenepo nkumayankhula zauchitsiluzo ?,.

  4. Nkhani ndi yoti nthawi yatha pangatalike maka Zizacitika by force cox tixasowa cinacake nde pofuna kuthandixidwa tixasainilana basi poti tikufuna thandixolo kma pamaso pa Mlungu ndi tchimo ndithu musaganixe kti Malawi axakhalaso wabwino ayi apapa tikukwanilisa malembo basi kwabwino kukonxeka basi

  5. God will punish u soon just wait n see,Do u think ur clever than God? 2 Timothy vs 3 (zoipa zoopsa masiku osiliza )

  6. Wat a lyf dis world iz going to an end dis truuu heee kupha ayambaso kuloleza God must 4 give who have come wit dis plan ok and dziko ili panopa lili mmanja mwa satana devil iz controling dis world masiku osilizadi pakana pamenepo ayi iiiiiiiiii

  7. Mmmmmmm wapephayo ndani kma anthu inu zooona anthu simukuopa Mulungu mukungopanga zinthu zanu muli pheee dziko la mkaka ndi uchi ija lero ikupita kuti,,,mmmmm am ashocked

  8. So you mean evry stupid gallons who open legs should terminate.Iknow why pple are pushing for this cz we are a cursed generation.Kupha mwana wolumala ndmulandunso cz evryone has the right to live..who should decide this one shud live o die

  9. ABALE AMENE WAYAMBITSA MAGANIZO AMENEWO MULUNGU AMUKHULULUKIRE NGATI LILI BOMA LINGOYITANITSA MAPEMPHERO A DZIKO LONSE KWA 1 WEEK ANTHU TISALE KUDYA ( prayer and fasting) MULUNGU ATIKHULULUKIRE KUTI MVULA IGWE BWINO NGATI KALE

  10. chomwe ndaona anthuwa akufuna magazi ndie njira yopexera magaxio yawasowa ndie ndichifukwa akukamba dxinthu zopanda nxeruxi kodi iwowo anakakhala kut mai awo apanga ximenexo anakapexeka dxiko lampasi?? Dziko ngat ngat lakukanikani ndibwino kungovomereXa bass

  11. ndiyetikamanena anthuwopusa matitalowetsa ndale ayi koma kulikondadzikoli apapatiyeni tivomele kutitikusoweka utsogoleli chifukwa tsogoleli akanakhalapo sakananenazimenezi ndichimodzimodzi kunena kuti amalawi tiyeni tiziphana palibekusiyana komadziwani ichikuti chilichose chikuchitika chotsutsana ndi mulungu mukayankhamulandu pamasopake pamulungu

  12. Ndimabwerezabwereza kuti ngati dziko lithe msanga liyamba laku malawi kutha chifukwa anthu ake amakhala ngati ndi ophuzila koma taaaa mbuli zokhazokha zitsilu

  13. This is a very big sin before God! The Bible says Do not kill . NDE inu mulorelanji mchitidwe wakuphawu?? A Malawi think twice…..

  14. Signs of the times. Ngakhale apolisi asakumangeni pamene mukupha ana osalakwawo, koma kwa Mulungu mulandu wanu ngwachikhalire ngakhale pachedwe bwanji mukayankha ndithu because whatever you are doing here is accurately recorded in heaven and you will never escape this unbiased judgement. A creature becoming wiser than the creator. Cursed be all of you advocating for this foolish idea. Advocates of the devil.

    1. Read Exodus 20 Vs 1-12 Anthu Oipisisa Inu.Cenjelan,mvekan Padziko Lapansi Lino But Judgement Day Is Upon U.Mudzafa Imfa Yowawa!!!!Mzimu Wa Mulungu Ukudzudzulen.Repent And Be Babtised In Jesus Name,EMEN

  15. Ngati akufuna kuchepetsa chiwelengelo osadanda tingoyitana boko haram kapena alkaida adzachite nafe pang’ono olo tikangoyiyambitsa ndi mozambique tichepa nthawi yabwinoso

  16. Malo moti muzipempha mulungu kt dziko lanthuli liziyenda bwino km nlkhani zake za zoduka mutuzi kumbukilani kt ndinu olengedwa ndi mulungu

  17. Kodi..tiziti mwasowa ..zoti..mungatiuze.!!!
    Kapena ndi kuchuluka nzeru mopusa.
    Mmalo moti..mupeze njira yothesera mavuto omwe.!!
    Tili nawowa ndipamene..mukuonjezera mavuto ena.!!!

  18. Vuto ndlakut amene anabwelesa #democracy sanatiunikire bwno nde pano zimalamuro zomwe zikubwer pano nd zosusana nd #mulungu waku mwamba, kuphiphlisa kwake akut nd ufulu wathu, at kuteteza amayi mwanayo ai,muthu wazeru kumenyela ufulu ma #hule mot athandze ana oyendayenda town mu km ndkumakawathamangisaso #ndakwiya~nanu

  19. FUCK YOU,WHAT IF SOME ONE ALLOWED, HELPED YOUR MOTHER KUCHOSA MIMBA YAKO,WUD YOU BE SAYING SHT LIKE THIS,WE GOT PROTECT OUR UNBORN BABIES

  20. Ndikanakonda anthu amene akufuna lamulo limeneli akanafa mwachangu asanapange lamulo laolo. Chifukwa angayambe kutichimwisa. Akufuna adzitenga ana omwe achosao ndikukakhwima

  21. amene akutipemphayotu amayi ake sanawuzidwe kut amuchotse iyeyo…mchifukwa chake lero iyeyo akuti pempha kut iyeyo akhale omaliza ku mtundu wa anthu…nanga amene azawapemphhe amalawi pathupi azisamalira azachoka kwayani?

  22. Zautsilu Et. Akukatengela Ya Chiani Mimbayo. Kumanga Nyumba Kukapasula Ndi Chamba Chmenecho. Amenene Akapezeke Wochotsa Mimba Apolice Amumange

  23. Koma zowona munthu wa mzimu waumunthu nkumapana maganizo upusa ngati amenewa? chonde amalawi anzanga tiyeni timuope Mulungu osati mzungu..

  24. Jabulos At Work, paja Ndalama zikamalankhula chilungamo chimakhala chete, but what I know is kwa Mulungu kulibe kubisa kalikonse , inu amene mukupanga malamulo opusanu Amai anu akadaganiza zokuchotsani musadabadwe mukadakhala mulipo inu? Mukunena kuti ayi dziko osamaendetsa ndimalamulo Atcharitchi mmmm Shame on you! The Bible Said Akapanda kumanga Dziko Yehova Olimangayo angomanga Dziko chabe, Mukufuna kundiuza kuti inuyo Ndi Mulungu wanzeru ndiinuyo? Oimba wina wake adaimba nyimbo akuti Ena akaphunzila Sukulu yomweyo Amasanduka nayo Mikango nkumapha Anthu nde mwaoneka yapa mfiti za anthu mikango yolusa, ndalama zake ziti? ndipo Sukulu Yake iti? mwandinyasa kwambiri . Musamutenge Mulungu ngati James, kapena ngati Amalume anu, Milili ili mbweee mukufuna kuonjezela ina? anthu inu mumauluka ndithu kutamba Mulungu Achite nanu ndithu Ndipo akuonetseni polekela!!

  25. Hillary Clinton and Obama supported this shit. Trump akukaniratu nyasi izi. Ma NGO amene munapeza mgodi pa nkhani ya abortion, gay & lesbian rights munyera funding simuyiona. Trump demurs this shit.

  26. Dziko ndi zintchito zake.
    Lero m’malo mowauza anthu zinthu zomwe zili zolondora mwati ai kma tingowapotozeratu.
    M’malo mowalangiza kti asiye chiwerewere mwati ai kma mukapezeka kuti mwatenga mbimba inu kaichotseni.
    M’malo mowalangiza atsikanawa kuti say no to sex b4 marriage inu mwati ai kugonanako vuto kulibe kma mukapezeka kuti mwatenga mimba kaichotseni.
    Anawatu ngati akusongonekera vuto ndinu.
    Chovuta ndichani kuwauza zoona zeni zeni atsikana athuwa.
    In as far as I knw,atsikana athuwa kuwauza kuti tsiyani chiwerewere ndiye kuti tikuwalakwira,this is nature and u cnt run away from this fact.Kma atsikanawa akuyenera kuuzidwa kuti kugonana mukandali ang’ono,kapena kuti musanakwime sikwabwino.
    Mkuwapasa sizanso zomveka bwino monga,,,kutenga mimba ya patchile,zomwe mapeto ake ndiye kuti mwazionongera nokha tsogolo lanu,kutenga matenda zomwe zosatira zake ndi imfa.Kusiyira xul yanu padela zomwe zosatira zake ndi ndizokuti mwazionongela nokha tsogolo lanu.
    Atsikana athuwa akuyenera kuuzidwa zoona zeni zeni zokhuza kugonana.Akuyenera kuuzidwa kuti u can only enjoy this thing wit ur husband and by then sizakhala kuti zikuchitika the way God Almighty intended it to happen.

  27. eeeeej,koma yah!mulungu akanthadi,ndiyo mwapeza njira yachidure yochepetsera chiwerengero cha amalawi?zopusa basi akadakuchotsani inuyo mukadakhalapo?stupt,kukwatirana amuna okhaokha tidakukanirani,kugwiritsa ntchito macndm sizikuyendaso swt mpepala,mwayamba kugawa macndm kwa ana asukulu aprimry takukaniraniso tsopano mukuwuza amalawi kuti aziphana,cholinga chanu ndichani?vuto lokhala ndi atsogoleri osapenphera ndilimeneli.

  28. Izi ndizomwe tiyenera kuzimva ndipo sizinati uku ndikuyamba chabe,wamzeru samachotsa mimbayo,chifukwa ndikupha komwe Mulungu akudana nako.

  29. Ndipo amene wabweresa nzeru, ndi maganizo amenewa aona ukali wanamalenga kumwamba ndithu; ntawi yakusodom ndi gomola mulungu ananyekesa mzinda cifukwa camacitacita asatana devil, ngati amenewo, Ndipo ndikucita kuonerathu kuti akufuna kuthesa cikristu kuti Satanism ilowerethu msanga kuti magazi aana osabadwa zikhale nsembe kwa mbuye wao satana kuti aapase zimene Yesu anamkanila kumpembeza or kumgwadira, Maufumu ndi maulamuliro ampamvu zakumdima ngati zimene tikuziona ndikumva apa lerozi.

  30. Tikanakhala kuti timaopa mulungu,sibwenzi ganizo limeneli litabwera.tchimo likamachitika kwambiri tikumafuna kulivomereza ndilamulo. Amene sakumafuna kukhala oyembekezera azipewa kapena asamapange.kugonana kumasowa kumasowa kukhala responsible.

  31. Tikanakhala kuti timaopa mulungu,sibwenzi ganizo limeneli litabwera.tchimo likamachitika kwambiri tikumafuna kulivomereza ndilamulo. Amene sakumafuna kukhala oyembekezera azipewa kapena asamapange.kugonana kumasowa kumasowa kukhala responsible.

  32. acahalichi kunena chilungamo sayenela kulowelela zandale potidi nkhaniyi siyachalichi koma yaomwe amayendesa dziko…nde achalichi sayendesa dziko koma andale….achalichi udindo wawo ndiwowuza anthu awo kuwawuza zomwe zikhulupiliro zawo zikunena pankhani yakuchosa mimba…ndipo izi zizapangisa kuti ochosa mimba achepe poti alichikhulupiliro chachikulu…..kwaine kulakwa kuchosa mimba koma anthu akuchosabe…izi zandale avomeleze akane kuchosa mimba kulakwa ndipo sasiyaso kuchosa mimbazo….ndipo kufa sasiya poti ku SA kuno amalola koma nako amafasa kamba kakuchosa mimba.

  33. Kupempedwa ndi boma kuti mtundu wa amalawi aziuthera m’mimba shame!!! Boma lopanda nzeru sindinalionepo ngati limeneri.

  34. Ndikunenetsa kuti amene avomereze zopusazo ndithu kumwamba kulowerelepo,kotero kuti thambo lakuda ligwe pa iye,ndikupemphela ndimphamvu zochoka kumwamba

  35. akayambe Kaye amai ake a amene wapemphayo kuchotsa mimba ya iyeyo,akakamuchotsa iyeyo nde abwere ku Malawi adzatiuze tidzichotsa mimba…atleast I’ll be convinced

  36. Pang’onopang’ono satana wayamba kuyenda ndi mwendo yonse ngati dziko la SA zovetsa chisoni kwambiri,Mulungu tithandinzeni

  37. I will say something on this anyone who share blood GOD HE will punish him so if u want punished with GOD you can do it you people of GOD this is what devil want he want all of us we mast go to heaven he want to go with us to hello but we got choice so make your choich in JESUS NAME I PRAY amen

  38. Amuthalika.muziganiza bwino2, akanakhala amayi anu analola kuchosa mimba ya inuyo kodi mukanafika pamene mulilipo .Kodi koma simukudya chamba? /nyaupe or pinch……….

  39. palije zeru.in malawi w hv rght 2 lf sono abotion z nt violtng ths rght?cz abortion z killing of un born baby may b unborn baby hasn` t any rght.to me ndi ngazomera yayi.

  40. vuto ndiloti azimayiwo azichotsa mimba za ana ot akanazakhala azitsogoleri abwino aphindu pa chitukuko cha dziko lathu ndikumasiya mimba za ana osalongosoka mbava komanso zitselekwete ngati azitsogoleri alipo lerowa

  41. kusowa dzocita mlungu anat usaphe welenga pamalamlo omwe ananen. kucit kupang budget amakumvutitsan cithandzo? akanakhal amai ako akanapha ie bwedzi thandizo akulipedza? asa

  42. A Malawi apemphedwa kuti akhale anthu omvetsetsa pa nkhani ya lamulo lokhudzana ndi kuchotsa mimba.Malamulo ololeza kuchotsa pakati akufunika ku Malawi.Malingana ndi mkulu wa bungwe loona kuti palibe kusiyana pakati pa akazi ndi amuna, la Gender Coordination Network, Mayi Emma Kaliya, a Malawi akuyenela kukhala anthu olola kuti lamulo limeneli liikidwe.Pakhala pali mpungwepungwe pakati pa a Malawi pamene ena akufuna kuti amayi aziloledwa kuchotsa mimba koma ena, maka atsogoleri a mipingo akukana kuti ayi. Iwo ati chifukwa kuchotsa mimba ndi kupha. Koma onse ogwilizana ndi kulola kuti amayi azichotsa mimba ati dziko silingamalamulidwe ndi malamulo a Chalichi. Enanso akuti mchitidwe ochotsa mimba umachitika ndi kale koma mwa njira zosayenelela.“A Malawi akuyenela kugwilizana ndi lamulo lovomela kuchotsa mimba ili kuti titeze amayi ndi asungwana amene akufa Kamba kochotsa pakati,” anatelo a Kaliya.A Phungu a kunyumba ya malamulo akuyembekezeka kukambilana za nkhaniyi.

  43. Abale malawi ndi dziko lowopa mulungu why doing so?yehova mulungu wanga menyani nkhondo anthu mdziko muno akanali mnthawi yakusadziwa.

  44. dzimen mkupang ndzanu, mzapedza kt wacotsa mimbayo unali ndi mwan yokhay amene watay. abale inu ndzoona kumalimban nd mlungu? lnenso ndkupemphela kut mlungu yemwe ndkumziwa akukanthen.

    1. Zoona mulungu awakanthedi,akutionjeza kwambiri,asakambilaneso nkhani ngati zimenezo,kod akufuna azikambilana zichani?zopusa!

  45. ooooh my God mchifukwa chake chichonse chilichovuta mdziko lathuli mvula kuvuta njala yosatha umpawi wadzaoneni chifukwa chamachimo….Malawi walero wavuta basi

  46. Kodi inu @malawi24, sukulu yake munapita ndi iti mukulephera kupereka uthenga osakwanira komanso ofuna kusokoneza anthu? Nkhani ndiyokuti akufuna kuvomereza kuchotsa mimba mwa malamulo osati azilola amayi kuchotsa mimba ngati anthu ndikale lonse samachotsa mimba.
    komanso bwanji osangopewa kulekana ndikutaya ana osalakwa?

  47. Wayambisa ndani bwanatu ulendo wanu womwe mudapita ku usa wayamba kutiophya kenako tinva zoti ana nzimayi akachila ana aziwasiya kuchipatala ngati kuno ku joni akatelo aziwaika ziwanda ife ayi takukanani kupha toto kabwezeni.ndalamazo

  48. Inu zisiru kwabasi zikusiyana bwanji ndikuphana,kodi amalawi mukufuna dziko lanulo lifike pati pati kweni kweni,inu zoona mungamalankhule pamaso pa mlungu kuti anthu azitaya mimba.Mwa ndi lirisa ndipo ndikupempha kwa mlungu achite nanu moyenelera nonse amene mwatengapo gawo pankhani yokupha ana osaziwa kanthu ndi osalakwawa Dzikomo

    1. Man mphatso zandikhuza kwambili chifukwa ineyo ndili ndi moyo makolo anga anakaganiza zokuti anditaye sibwenzi ndikuona zomwe ndikuona zokoma ayi

    2. Zizindikilo zamasiku osiliza izi anthu akumalolela kumachita chithu akuziwa kuti ndichilakwika chifukwa cha makobili.kodi kaliyayo mayi ake akanakhala ndi ganinizo lopusali akanakalankhulila kuti mbwelela zakezi?

  49. Kuteloko, alola kale chifukwa chandalama apasidwa ndi maiko ena, mabungwe ndi Papa. Boma linavomeleza Zamatanyula apa akuti kuchotsa mimba, mawa ndizina. mabungwewa afuna kulowasta zausatana kuno with exchang of money. wk up mw!

  50. Amalawi tsopano asowa zoti apange ndiye kumangoganiza zomachotsa mimba.Nanga tingati pali zeru pamenepa Kkkkk kumaganiza mozama amalawi inu muli ndi moyo pano bwanji akanakuchotsani nthawi yomwe muli ndi mwezi maganizo amenewa mukadawatulutsa? Ngati kutenga mimba inuyo kwakutopetsani katsekeni osakhala kumawuza anthu nkhani zopusa ngati zimenezi. Palibe mimba yomwe imabwela iwe mwini usakudziwa,Ganizani zoti zitukule Malawi.Mukunva

    1. Zoona madala akuganiza ngati anachita kugwa kumwamba aiwala kt akhalako mimba akufuna kuchotsa panozo. Chodabwisa akufuna azichotsa zaanthu ena ngati azimawo ndi azikazi awo angachotse

  51. Zopusa zimenezo akuteroyo mwanayo amalenga ndiyeyo zochitsilu basi Malawi sazathekanso kumangomvela zilizonse zoti munthu akamachotsa mimba amatha kufa simudziwa zamanyi basi

  52. Mukamati akuloredwa kuchotsa mimba amakaniza ndindani popeza zake zonsezi anthu mimba akhala akuchosa alipo anamangidwapo BLM NTchitoyake yaikulu mesa ndiimeneyi nde mufuna ukambachani apa

  53. palibe zochotsa mimba anthu akamakwatana amakhala akudziwa kutii akhoza kupatsana mimba.paliibemimba yobwera mwangozi ndie kungosiya kukwatanako,fwetseki mutitukwanitsapo apa.

  54. Zayamba!Muganiza Papa Ndikumuziwa ineyu!Angapeleka Chithumba chamakobidi opanda profit yake’kkkk Muyenela Kupeleka sembe ka. Nde Malamulo Amakatenga Kwa papawo Ndamenewa Zina zikubwela apa mphoyambila chabe.

    1. If this issue of abortion is supported by the Pope let God himself punish him BUT if You statement is false what do you think will happen to you?

  55. Kuchotsa mimba? Jesus plz come quickly. All things that you said don’t do, one by one are now changing in favor of the devil not you. Very pathetic. God will judge you one day

Comments are closed.