Man arrested for killing elephant

Advertisement

Police in Machinga have arrested a 31 year-old man for killing an elephant at Liwonde National Park in the district.

Machinga police spokesperson Davie Sulumba identified the suspect as Elifa Makhwele from Liwonde village.

“It is true that we are keeping in custody Elifa Makhwele aged 31 for killing a male elephant at Liwonde National Park” he said.

elephantsAccording to Sulumba, Makhwele together with his two friends who are at large went to the protected area and killed the elephant.

Park workers did not manage to catch the poachers but they recognised the suspect and reported the matter to police.

The law enforcers then raided Makhwele’s home at 3am on Friday and they arrested him. The police however are still hunting for Makhwele’s friends.

Elifa Makhwele who comes from Imani village in the area of Traditional Authority Liwonde in Machinga will appear in court to answer charges of poaching and illegally entering a protected area.

Advertisement

68 Comments

  1. Munthu ndi nyama chofunika kwambiri ndi chani? Kodi mukuziwa kuti mulungu anaika ulamuliro mwa munthu kulamulira nyama osati nyama kulamulira munthu?

  2. apolicewa nawonso ndi agalu achabechabe .tell me how meny peaple the dea about elephart and how meny elephat do you rest ?? zapha ndi kuwononga zinthu zaanthu kumachinga so what u do kupusa basi shoopeat give him a barow

  3. Apolice amzanu,Khotekhote mazengera, Namisisi adaba matumba achamba 50 kusalima uko osawamanga bwanj? Pano angochinda mahule alipheee… Uja wabetsa mfuti kamba koledzera uja omsamanga bwanj? Mumaoneka anzeru zkakhala nkhan zaanthu ena, zambanja mwanu nde kukhalira, Njovuyo ikadamupha Elifayo mukadatan? Mdatopa nanu agalu inuuu…

  4. Osango muombela n.manja kuti ndi dolo waphayo bwanji koma njovu ikapha munthu nde ziiii sizimamangidwa bwanji ndindiwo imeneyo ndemuka mumanga idzuka njovu yo ndinthawi yoka longo sola iwola nthawi muku musungayi amati gulitsa motchipa akapha nyama ameneyo zimasiyana ndiyoti takagula ku msika

  5. Koma akadapha albino ndiye mukadamusiya,kunena kwake mumati ziribe umboni koma lero mpaka pano mwana sakuwoneka anthuwo ali free.Wapha njodvu lero lino akugwira ukayidi mmmmmm shame malawi wamoto machinga eeeee

  6. ukapita kuchipatala ukalandira mankhwala angokupatsa panado ati enawa ndiodula kaguleni kuprivate,kodi ogulitsawo amawatenga kuti?amawapatsa ndani?bwanji osawamanga iwowo?koma mulibzy kumanga anthu oti mfutizo mudawapatsa nokha lero mukudabwa mukuti atiphera nyama!nkhani ndiyoti dealyo simudagwirizane mwina sadakunyemereni,kuthamangira kumanga oba nkhuku koma acashigate aliphe kudya misokho ya amalawi,kumvetsa chisoni kumalawi

  7. Apolici unu mulibe mzelu bwanji osamanga iba ndalamawa akapolo awanthu inu apolici aku mw opusa mukungofuna kutchukila bas mbuzi zapolici

  8. Nkhani yabwino wachita bwino mumafuna kuti Njovuyo imuphe.Mukanayimangakuti ikasewenze jeri komanso ndi ndiwo imeneyo athu achape nkamwa.Mumumasule alibe mulandu ameneyo

  9. Why arresting him for Killing an elephant? He must be very energetic and courageous, in the bible Samson killed a Lion who arrested him? This other boy called David also killed Goliath who arrested him? Instead all these guys were given a hand of applause and given special titles, so our man in Machinga must be given a gun and employed as a Game Ranger.

  10. Igt Surprised with this gvt they r’bzy arrest Innocent Pple,he kill an Elephant he want 2sell Ivory is money,wy dnt Ugo arrest those Cashgaters out there’Muva Apolisi Kwa a Vumbwe amanga anthu 40 nyengo ino ya X-mass kamba koyenda Usiku,zaziiiii.

  11. kunziwa kumanga opha nyama koma oba misokho ayi pot nawonso akupangitsa kut makhwala azisowa nzipatala za ziko muno kupangitsa abale ndi anasi athu kufa ndai matenda oti akadatha kuchila apolisi inu mukhale serious mwanva

    1. Njovuyo anaipha kumalo otetezedwa ku park siinali mmuziyi kut iphe munthu mukanawerenga kaye nkhaniyi man…
      .
      Mukut zanziii simuziwa maiko aanzathu ngati South Africa amapeza chuma chambiri kaamba ka njovu ?? Muziwerenga kaye nkhani musamangopanga reply nkhani musanaiziwe…

Comments are closed.