Mkwatibwi athawitsa ndalama za pa pa ukwati

Advertisement
Money currency

Mkwati wina m’dera la mfumu Musisita m’boma la Nkhotakota walira ching’ang’adzi mkazi yemwe adakwatira naye atathawa ndi ndalama zomwe adapeza patsiku la ukwati wawo.

Malingana ndi mfumu Masisita, Bamboyu adakwatirana ndi mayiyu mulungu wathawu koma bamboyu adazizwa ataona kuti mayiyu pamodzi ndi ndalama zomwe adapeza patsiku la ukwati wawo sizikuoneka.

“Padali patangotha masiku awili pomwe mkuluyi adadziwa kuti mkazi wake wamuyenda njomba pozembetsa ndalama nkuthawa nazo,” Mfumu Musisita Wauza Malawi24.

“Bamboyo adayesa kufufuza komwe kuli mkazi wakeyu koma mpaka pano sakukupeza,” adaonjezela mfumu Musisita.

Money
Ndalama zathawisidwa.

Mkwati ndi Mkwatibwiyu onse ndi a m’mudzi mwa mfumu Musisita, Mfumu yayikulu Kanyenda m’boma la Nkhotakota.

M’mudzi omwewu wa mfumu Musisita, M’busa wina wasiya ubusa kamba kosankha kukhala ndi mkazi wachiwiri.

Malawi24 yapeza kuti m’busayi yemwe ndi wa mpingo wina m’dera lamfumu Musisita m’boma la Nkhotakota adakwatira mkazi wachiwiri zomwe zidali zotsutsana ndi malamulo a mpingo wake.

Malipotiwa akusonyezaso kuti izi sizidasangalatse akuluakulu ampingowo omwe adamufunsa m’busayi kuti asankhepo chimodzi pakati pomusiya mkazi wachiwiriyo ndikupitiliza ubusa kapena kusankha mkaziyo ndikusiya ubusa.

Akuluakulu ampingowa adazizwa ataona kuti m’busayi wasankha kusiya ubusa ndikukhalabe ndi mkazi wachiwiriyu.

Pakadali pano m’busayu wanenetsa kuti sangamusiye mkaziyu wake wachiwiriyu.

Advertisement

211 Comments

  1. kkkkkkk mkaziyu mwina amawonerera kwambiri Nigerian movies, ndiye imeneyi ndi real action.Mwina akukawengera kaye kutchire kuwopa akuba abwera nazo madzulo ano !!!!kkkkkk

  2. Yoweta sagula pansika,ndikukhulupilila kuti wakupasa phunziro.

  3. Yimwi Kaka Koma Mdamujiwisisadi Dada Uyu Kapina Mdagula Pa Msika? Nimu Vikhalira Mkatola Nakudya Mfulumira But Its Ok Life Goes On Chafukwa Simwi Woyamba Wambiri Wadakumana Nazu, So U Better Pause And Ask 4 D Time Inangu S O R R Y !!!!

  4. If interested all cute ladies available in this group who needs a guy to give them good sex and this includes all sugar mummies or just older ladies but should be smart and ready to spoil with money inbox or call on 0882926882 same line hit me on whatsapp, love you

  5. I am here to give my testimony about a doctor who help me in my life. I was infected with HIV virus in the 2010,i went to many hospitals,churches for cure but there was no solution out, so I was thinking how can I get a solution out so that i cannot loose my life, I lost everything I have my husband run away from me and also took my children along because of my sickness. One day I was in the river side thinking the next step to take if it is to jump into the river so that I can loose my life totally or just think where I can go to get solution. so a lady walk to me telling me why am I so sad and i open up all to him telling her my stories, she told me that she can help me out that’s the reason she normally come here to help people so that thy can be cured because she was into this problem before, she introduce me to a doctor who cast spells on people and gave me he number and email so i called him and also email him. He told me all the things I need to provide and also give me instructions to take, which I followed properly. Before I knew what is happening he called me and told me that i should go for test which i did to my greatest suprise the result came out nagetive, am so happy right thats why i decided to share these with my brother and sisters that is passing through pains contactthese great man he will help you through whatsaap +2348162447651

  6. akazi amasiku ano mtima pandalama basi zabanja ndinyambo chabe,safuna tsiku kulowa osamwa tiyi amayesetsa kaya ndiwa chimanga chokazinga bora ziyende zikapanda kutero mapeto ake akuthawa

  7. kumachenjela pa town n’dala,nkazi osamamukhulupilira ngati FMB pa nkhani ya ndalama apa ngongole ubweza bwanji ?

  8. Haaa dzoona wathathawirsadi. Ndalama zija.. Haa wandililirsa ku usi zedi. Haa ine kumati ndapeza. Yanga njole yondipukuta. Minsonzi pathawi yamavuto. Haa wandionjera. Minsonzi yakhani khani masaya anga. Haa kodi ndilowera kuti. Haa wapitadi wachikondi chabodza uja. Haa uyu yekha waswa mtima wanga. Haa kundipyopyona konse kuja inali plan. Haa zoonadi iwe wekha wawina..Haa sindibweza choipa. Koma tizaonana pa siku la chibaluwa

  9. A good wife who can find? she is far more precious than silver and gold; her husband trusts her. she does him good, but not bad all the days of her life.

  10. nkhani iyi ndiyongopeka sizoona izi. unali ukwati wa mpingo wanji umeneu? mkazi wachiwiri mpaka ukwati lol mbusa wa church yanji osanena apa?

  11. Uuu uyu dziko lamuziwa kuti awawidwa …..but story makwatirakwatira anuwa mwakwatisa mbava achimweneeee mumalo moganizira honey murn ayamba ndlama kut zapitaaaa

  12. She wasn’t serious with the marriage, finally she get what she wanted, she wanted that money most not that man, she was after money, thats what happens when you are forcing a prostitute to be your wife!

  13. Azimayi iiiii kutengeka wina akuwona kuti uyu ndi m’busa ndipo ali ndi banja lake koma nonoloo pomweposo kodi bwanji kusaugwila ntimawu?

  14. Azimayi ambili akutenga banja ngati bizinesi, chikondi chinatha kale, angofuna kuzikundikila chuma basi kumangomupusisa man …….

  15. Kaka namwe vibwataka mwapanga ivi vitinyozetsa kwambire,akaze amasiwano safunika kuroromwa yaye zotchatila zake mvinevi.mpiti kwawo mukayabwi akabwezi mteleshede osewo kuphatikizaso nkhuko yakamoongo akapheleki

  16. yoweta sagula pamsika!mwinatu nkutheka anamutenga kubala!mamuna pamafunika upange kaye chibwezi, kumufufuza mkazi kwao makhalidwe ake then ukwati.mani munadya mfulumira.

  17. Tiyeni tikomente Chichewa guys Chifukwa nkhaniyi ndi ya Chichewa kkkkkkkk Sitikufuna kuwelenga zizungu zanu zozungulira mutuzi kkkkkkkkkk Iya nanga tiname hahahaha , Chizungu chinechi atakumvani eniwake azungu akumangani Sure !

  18. Hahahahahaha Si ku Ngala kodi. Za Chitonga ndi zomwezotu. Tulo mumaso ngweee Koma tsopano aziti ife a Tonga ndi ochenjera. Kuchenjera kwake kuli kuti tsopano apa? Kuchenjera powedza nsomba basi pokwatira ndikusunga ndalama zaukwati tulo.

  19. Zakuba zilibe zilibe tsogolo ,,if u take from universe no matter how long it might take the universe will take it back from u,,

  20. sadalakwitse mkaziyo pajatu nthawi zambiri maukwatiwa amaluza ndi akuchikazi.

  21. Siwa Chikondi Ameneyo Chikondi Sichocho Nijuleli Menelo Achinyamata Tiyeni Titengepo Phuzilo Mawa Ndife Chenjelani Achinyamata

  22. Many ways of getting rich, but dis is rediculas, mwanyozetsa boma langa. Man muziona mkazi omukwatira….mukayamba chibwezi mukanamudziwa koma madulira ndio akupwetekani bro. Sorry.

  23. mwina anali ndipassport imamusowa transport fee ndekuti basi ameneyo wadusa ali kuno ku SA…paja ku Nkhotakota safupa zambiri zonse zathela munjira…chongofunika abeleso ena pano pafumbi labwana Zuma.

  24. Akulila ngati ndalamazo ndi zake oyenela kulila ndi amene amasupa ndalamazo zilingati kumuwuza mkazi kuti choka pa nyumba panga pano chonsecho ndi pa rent

  25. Eeeetu Azikazi amasiku anotu maso Ali pandalama osati chikondi chenicheni ayi, Ngati ndalama yavuta uzaona behaviour ya mzimayi yayamba kusinta mbanja. Sono apopo zaonetserathu kuti sanali mkazi ofuna ukwati ayi koma ndalama. And wazipeza.

  26. Nkhaniyi amene walemba akanayilembaso. Sindikumvapo kanthu . Pali nkhani ziwili zosagwrizana.

Comments are closed.