Ntchito ilipo pa mayeso a Fomu 4: ati a MANEB azifunsa kuyambila zinthu za Fomu 1

Advertisement
exams

Kuthetsedwa kwa mayeso a Fomu 2 kwabweletsa mavuto ambiri pa ana amene asiya kulemba mayeso amenewa.

Mavuto awa adza zitadziwika kuti bungwe loyang’anila za mayeso m’dziko muno la MANEB lili ndi ma plan oti tsopano mayeso a Fomu 4 azikhala ndi mafunso oyambila zimene ana aphunzila Fomu 1.

Malingana ndi chikalata chochoka ku bungwe la MANEB, mayeso a Fomu 4 tsopano azikhala ndi mafunso a zinthu zones zimene ana aphunzila ku Sekondale.

exams“Paja kale lija timangofunsa za Fomu 3 ndi 4 basi pa mayeso a Fomu 4, koma tsopano zinthu zasintha. Pano tizifunsa zones kuyambila za Fomu 1,” atelo a MANEB mu chikalata chawo.

Zimene a MANEB alengeza zadzetsa tsemwe pakati pa a Malawi amene ali odabwa ndi zilinganizo za MANEB.

Anthu ena amene ayankhula ndi Malawi24 ati zimene akukamba a MANEB ndi zovuta kuti zichitike.

“Koma ngati amavuta mayeso a 4 aja zinthu za Fomu 3 ndi 4 basi, ndiye akanene kuyambila Fomu 1? Apa ayi ndithu apaunikile bwino,” anatelo mkulu wina pothilila ndemanga.

Advertisement

100 Comments

  1. Kkkkkk nzeru zatha, instead of making plans to develop the country and create jobs ur busy abolishing Jc hahahahaha, even dogs and cats are laughing at u baba hand over the power if u fail to rule the country and I hope soon u will abolish Msce and next target is University, I never seen a government like this in this planet which kills Education hahahahaha don’t make me laugh.

  2. Ngati mphunzitsi amaphunzitsa subject imodzi basi what about anawa aziwelenga bwanji kuyambira za form one mpaka 4 kkkkk chifukwa zinthu sidzikusitha Ku mw

  3. Koma Kunali bwino akadazisiya kuti mayeso azilembedwa .koma kusitha ndiye kuti mitu yawanafe isithaso aziti oti tizingolowa

  4. i think this Dpp goverment is afraid of other graduates they want to maintain their current positions as far as education is concerned this government has done nothing apart from raising the tuition fee.For instance polytechnic students are just moving up and down pamapeto munthu akapalamura akuti pereka 3million nt only poly zomwe zikuchitika pa mzuni pamapeto timva aseka school.Malawians i cry for u becouse how can we talk about social-economic development if our children are at home roting with ignorance? this is not point of children working hard but this regime wants that iliteracy level should go higher so that akamayakhula chizungu tiziti inde bwana just becouse we can speak english what a pity!

  5. i feel very sorry for my beloved mother land(nyasaland)nothing is never been stable since when Dr H.kamuzu banda decided to let it go(died)today this and that !!!!,tomorrow,…. shit,here we go back again.simaphunziro okha,even vacancies,monga police, prison,Malawi army, teaching. amati tikufuna anthu 4 thousand, end of a day,anthu 3 thousand amakhala ana kapena zibale za mabwana.anthu 6 hundred odisha ndalama,the least 4 hundred akuti yathu imeneyo tinyosolelane,kkkkkkkk. do you think mphawi wa ku mudzi apa pali chake??? not only that, even ma research projects abwino amalembana okhaokha,ife timangonva atii kunali project ya(……)kunva zothaitha shaaa!!!….lero kuli atiii,Ulimi wa nthilira,one village one project, Green belt, atii Ulimi ya mtaya khasu hahaha….nde kutikodola zisanayambe ndi komwe,cholinga tizilima kwambiri kuti iwowo azidya kapena kutigula pa mitengo yotchipa.hahaha ameneyo nde malawi walero.

  6. i feel very sorry for my beloved mother land(nyasaland)nothing is never been stable since when Dr H.kamuzu banda decided to let it go(died)today this

  7. kusowa chochitatu uku,akulu akulu ndithu round table discussion,mataye kuno suti zili pholipholi kugwilizana zimenezi,ndiye chimodzi modzi wana kusewela pamchenga,hahaha malawi sazatheka.

  8. Ooh dat plan mu malawi zibwezeresa umburi wazaoneni bola zinthu zikadakhala ngati kale momwemuja bwanji dat system its not gud many pple will drop at xul 4sure

  9. Hahaha ..thats what i really 100% know about malawi ….though they will do that we dont given opportunities to work with that msce paper ..imagine ayoung person from malawi deserve to spend 16-18 years searching for better education after all he has all the papers from university umva kuti ulembedwe ntchito u must have 4-8 years experience ….rabish.where do we gate experience while you are not giving us opportunity …..marks zero MANEB

  10. Kufuna kuchulukitsa umbuli pa Malawi. I wonder what the government is doing about this mwina poti ma mp ambilinso xool yawo imakhala yo pelewera. Kodi nfundo imeneyi can’t be contested in a court of law????? This is just too much.

  11. Nanuso a Malawi24 mumasowa zopanga post eti? MSCE amafusa from primary to form4 ndie pali zachilendo apa? a Malawi Vomelezani kusintha dzulo silero mesa kale anthu amkalemba mayeso a boma mu std5? zilikoso lero? it was only Malawi left behind wth JCE, Osaopseza ophunzila MSCE izifusidwa mwa normal like mmene zimakhalira (Malawi24 unproffessional web pages) Muziposita zakupsa osati mbwelera madzala mphuno okhaokha ndi ufulu wanga kulankhula zakukhosi (SECTION 35)

  12. Delta Hotels Toronto,is Currently recruiting able bodied workers from all over the world to fill in the following vacant positions such as:Room Services, Hotel Receptionists, Kitchen References,Hotel drivers, Pool Management, Gardeners, Security Services etc….Application lasts from now till 30th November 2016….for Applicants in America/Europe/ Asia kindly whatsapp miss Lisa on +16474920576 and for our African applicants whatsapp mr Josh on +221708781126 for guidance. …Wish you all the best of luck and will be delighted to meet you all here soon….Thanks….

  13. koma szabwino, kuymbra primary mpaka scondary 4m 4 otsaziwa kuynkhula english. amen apangzimenezo potzao zidayenda enafe mmmmm kulilabac.

  14. Boma-la-democrancy-eeeee-padziko-lamalawi–palibe-chomwe-chizamange-malawi-wabwino-mumabweretsa-ndondomeko-ngati-mukufuna-kukonza-koma-kulikuononga–kamuzu-adatsogolera-dziko-lamalawi-pofuna-kwathandiza-amalawi-pamaphunziro-kare-wa-standard-4-amalankhula-chizungu-lelo-mpaka-form-2-ena-chizungu-kulephera-chifukwa-chiyani-Akuwunduna-wamaphunziro-zambiri-mwakwefulakwefula-kodi-mukufuna-akutameni-poti-ndinu-zanu-zidayera-kare-?

  15. Very sad. After 52 years of Independence authorities in the ministry of education have not yet explored the standard curriculum for high school students.

  16. Ine ndimayesa mutiuza kuti mayeso abwelere a standard five koma mukuthesa jce ukunama iwe wazipeza zimenezo zizabwelera!kumbukila mchimwenewako za flag inabwelela !
    Anyway ur moron stupid chavumbwah President

  17. ngati work ya 3 4 ana amalakwa ndie akaikenso 1 2 zoona? kodi dzikoli likupita kuti? ndani ochuluka nzeru akusocheretsa anthu anzeruyo? dzuka malawi dzuka

  18. POYAMBA AKALAKWA A4 AMABWELEZA AMAYAMBA M3 NDIYE PANO U MIN KUT AKALAKWA AZIYAMBASO MU 1 OR W? JUST STUPID POOR PPLE%

  19. Maphunziro a ku malawi nawonso sadzatheka,tangoganizan kumalimbana ndi ma parts a dziwala pomwee anzanu ku japan akupita pa tsogolo ndi science.Nde akakhala ma sukulu akwathu ku nkhotakota kumangotuma anaa kut akatenge nsomba akut afuna kumanga experiment
    asaaaaaa

  20. Umbuli ukupitilirabe kwathu kuno Malawi sizathekaso bas bola amene mnaphuzra xul zakale mumanjoya ndmaphuzro nt nw ndiumbuli okhaokha bas

  21. Amangofuna kuwonongetsa ndalama za amphawi, ngati JC ena amabweleza katatu osakhoza ndiye from 4 adzibweleza kangati kuti apeze certificate. Uku ndiye kutha ma plan ndizamaphunziro

  22. Amaliza kufunsa mabuku onse aku senior? Ngat amaliza kufunsa osamangogawa ma certificate bwanj? Education is a serious thing but here in malawi we are not serious try and error idiots

  23. Kutha nzeru kumeneku! Anaphunzira zenizeni anaphunzira. Zikungomvetsa chisoni ife achimidzi we dont have a say. Ana athu sangatumizidwe kwaazungu kumaphunziro kma misonkho yathu ndiyo chosoweletsa olamulira. Tikakumana kumwamba basi! Ngati muli anzeru sandulikani ngati zakeyu.

  24. Kusowa Ndalama Ndichifukwa Chake Mwachotsa JCE, Ndkuona Ngat Kutha Kwa Maphunziro Kumeko Ndipo Umbuli Uchuluka. Ndkudziwa Kut Nyumba Imakhala Ndi Foundation. Foundation Ya 4m 4 Ndi JCE Sizanzeru Kuchotsa

  25. Mwachidule, it will be JCE and MSCE combined. This means in languages they’ll be more than 7 chich lit books and Eng 8 books, making a total of 15 books. The same in all subjects. Azidzayamba April mpaka July mayeso amenewa. Kkkk…

  26. uchitsilu basi mungofuna kulimbitsa maphunziro angalu inu kma2 zipangizo mulibe osathana kaye ndi ana akuphunzirira pa mtengowa bwanji?muli phuno pane kupusa basi ndi sukulu zingti zili ndi rabu or nyumba yosungira mabuku or kuwelengeramo?

  27. kodi munalemba JCE NDI MSCE ya ku jamaica eti mesa basic ya form 4 ndi 1 nde paliso vuto apa kkk vuto lomaloweza zithu mumaziona kuvuta a bas ndapanga unlike pageyi

  28. The problem is that Malawi Institute of Education (MIE), MANEB and Ministry of Education are really failing malawians. Why not revising the education system that malawi is following. Imagine how kamuzu made our education system! primary school is 8 years and secondary is 4 years and college is 4 to 6 years. if a pupil starts school at 6 and want to a doctor then must spend 24 years if he hasn’t repeated a class. So a 24 year person is grown up and is driven by money hence all he does is for fast riches. When given a job he start thinking of how to get rich and indulge in corruption hence the country doesn’t progress! One way of making a country rich is to reduce school leaving age. If students spend more time in school they become unproductive. Imagine the kamuzu academy system why not following it as other countries do (eg Zimbabwe)? imagine the age that a pupil leaves primary (14 years)! Crucial age of any child is between 6 to 12 so at this age of 12 make a huge workload for the kid to master (from Std 1 to 6) then should graduate to high school (by a national examination). At this age (6-12) expose the learner to various disciplines like art (fine and performing), science, business, modeling, designing, vocational skills, etc. Then allow the child to choose their discipline of specialty in Std 7 to proceed with it as a life time career up to tertiary level! But malawian system is a prison type of education system where every one follows an instruction to become no one knows. Why forcing every one taking subjects prescribed as medicine? imagine someone could have been a doctor but derailed because the chichewa subject just excited him and choose to be a teacher on the way! There is also another problem in malawian education system. There is a very wide gap between college and secondary work. eg science student will leave secondary without knowing any basic calculus but caught in surprise to find it in college algebra. Why not introducing it in secondary for ordinary maths not in additional mathematics.

    1. hahahahaha yea Jackie! Even the leaner doesn’t know whom shall he be. Even most of the college students learn a general degree not knowing who they will be. Imagine degrees offered at UNIMA the only professional ones are Bachelor’s of Education, LLB (law) nursing, Laboratory and Accounting, MBBS. The rest are general degrees

  29. kkkkkkk Malawi!!!! if we were failing to remember a yesterday’s lesson during our days will these youngster b able to remember a lesson of 4years ago?????

  30. kkkkkkk Malawi!!!! if we were failing to remember a yesterday’s lesson during our days will these youngster b able to remember a lesson of 4years ago?????

  31. kkkkkkk Malawi!!!! if we were failing to remember a yesterday’s lesson during our days will these youngster b able to remember a lesson of 4years ago?????

  32. thats so shamefull indeed as a Country.Seemz like the leaders of the country r ignorant in this Country. Think Think Twice if its one way of Saving Government money

  33. Hey u pple what are u saying? Frm my experience , form 4 involves all the forms ( 1,2,3 and 4) . Laziness pays not , they must be industrious enough , i rest my case.

Comments are closed.