A polisi akusakabe yemwe adapha mlaliki Wame

Advertisement
shadrek-wame

A polisi m’boma la Salima ati akusakabe yemwe adapha mlaliki odziwika bwino mdziko muno a Shadrek Wame.

Oyankhulira a polisi m’bomali a Gift Chitowe ndiomwe anena izi dzulo lolemba pa 31 Okutobala.

shadrek-wame
A Wame adachita kuphedwa.

A Chitowe ati iwo anakhazikitsa kafukufuku ofuna kugwira yemwe adachita chipongwe chimenechi ndipo anaonjezera kuti pakadali pano kafukufukuyu adakali mkati.

Mneneli wa a polisiyu anatsutsa mwantu wagalu mphekesera zomwe zikuveka zoti iwowo agwira yemwe akuganizilidwa kut anapanga chipongwechi.

Iwo ana izi sizoona ndipo anakanaso mphekesera ina yomweso yaveka kuti munthu oganizilidwayo anaphedwa ndi anthu olusa mdelaro. A Chitowe ati zosezi ndizabodza.

“Ife a polisi tikufuna titsutse mphekesera imeneyo chifukwa palibe yemwe wabwera ndikutitsimikizira kuti yemwe adapha malemu a Wame wamangidwa kapena waphedwa ndi anthu olusa, choncho zosezo ndizabodza. Chomwe tikudziwa ife ndichakuti kafukufuku ofuna kugwira yemwe adachita chipongwe chimenechi adakali mkati.”

Atelo a Chitowe. Iwo aonjezera kunena kuti anthu osiyanasiyana akuwatsina khutu momwe angampezere nkulu yemwe adachita chipongwe chimenechi.

Mlaliki Wame adapezeka ataphedwa mnyumba mwake mmawa wa la chisanu pa 28 Okutobala.

Ma lipoti akuonetsa kuti malemuwa adaphedwa ndi wantchito wawo yemwe adasemphana naye chichewa pankhani ya chimanga. Malemu a Shadreck Wame adabadwa mchaka cha 1940.

Iwo ankachokera mmudzi wa Mwanzalamba, mdera la mfumu ya ikulu Kambalame m’boma lomwelo la Salima ndipo aikidwa mmanda dzulo lolemba pa Okutobala 31.

Advertisement

67 Comments

  1. Akanapezeka mwa changu mukanati anthu akuthandizeni kupeza koma osati kukuthandizani kugwila munthuyo koma kumu otchaso ndemukana va zoti bwelani muzatenge phulusa kuno

  2. Delta Hotels Toronto,is Currently recruiting able bodied workers from all over the world to fill in the following vacant positions such as:Room Services, Hotel Receptionists, Kitchen References,Hotel drivers, Pool Management, Gardeners, Security Services etc….Application lasts from now till 30th November 2016….for Applicants in America/Europe/ Asia kindly whatsapp miss Lisa on +16474920576 and for our African applicants whatsapp mr Josh on +221708781126 for guidance. …Wish you all the best of luck and will be delighted to meet you all here soon….Thanks….

  3. Aja anaba ndala pa petroda Ku Lilongwe anagwida what more uyu mwazi wa munthu otsalakwa ukumutsaka.popano apedzeke satana amenei.

  4. Mhuu!! Mpaka kupha munthu wa Mulungu?? Ayitu Ambuye chitanayeni munthu ameneyu ndikumuzindikirisa kuti palibe chobisika pansi pathambo,

  5. by this way am sure simungampedze cz nayenso ali pomwepa kuwerenga ndi kuona ma post oterewa. mukumpanga encourage kukhala munthu ochenjera and kut athawire kutali. zinafunika kachetechete ife mudzangotiudza kut munthuyo/ anthuwo agwidwa. that’s all.

  6. We need to show love to one other.This preacher was not supposed to die like that and i was shocked to hear that.Please police do you your best to arrest the suspect.MHSRIP.

  7. Munthu anapanga zimeneziyu Chauta apange naye. Abale inu….just this same year mwana wao yemwe amawathandiza…he was residing here in South Africa…anapezekanso atamwalira mu bedroom mwake….sort of like anachitanso kuphedwa…in broad daylight. Mpaka pano his death still remains a mystery. A few months down the line….Bambo akewa also gets killed in such a brutal manner. The late son left six children who were apparently being taken care of by agogo awowa.
    Its so painful. May the Almighty Father God intervene…more especially kwa anawa. He is the only one who can take care of their welfare.

  8. LET HIM COME BACK AND EVEN SAY SORRY TO YOU.

    HERE IS HERBALIST AND TRADITIONAL HEALER TO HELP YOU..+27725564721

    Are you depressed ,feeling disappointed by your lover that he is changed you nolonger understand him any more then here is Herbalist Healer Shamim to help you flash away all those that are after him…

    Do you have any one prisoned but you want him be bailed out then come be helped,Are your kids not listening at you make them listen and understand you or be at good terms with them
    Am good in

    Bringing back lost lovers

    Stop Cheating and Breakups

    Flash away all those after your lover

    Students Pass Exams

    Bringing Back lost or stolen goods

    Iskhafulo or sea water

    Stop divorce

    Come for my manyonix Man power for your man hood

    Is any one hating you at work stop that

    Make your boss like you

    Get promotion at work

    protection spells to protect your properties

    Lock heart of your lover not to love any one else

    Ubheka mina ngedwa

    Remove or put iscitho

    Stop family misunderstandings and fights

    Come i cleanse your home

    Are you having Bad dreams come be helped

    Make your lover marry you and do as he promised you

    Are you having haunting spirits in your home i remove it away

    Make your lover feel you and get satisfied of you in bed

    Lock heart and his man hood be yours only.

    I have a cream which can make your penis big and strong permanent.

    CALL or Whats app +27725564721

  9. Munthu ameneyu agwida ndithu. Mulungu wa mphamvu amusaka munthu ameneyu mpaka apezeka. kukapha munthu wamkulu ngati ameneyu kuti iye apezapo chiyani?

  10. mvuto ndilakuti amalawi timalemphela kunena zoona potelo apolic amatenga nyengo pakafukufuku pakuti athu oipawa amadisidwa manyumba. koma kubukani kt mulungu salemphela patalike bwanji adzapezeka

  11. Munthu oipayu akuyenela kulangidwa ndithu akagwidwa,wapha munthu yemwe adali okondedwa kwambiri ndi anthu ndiponso mtumiki wa Mlungu yemwe amagwira ntchito yake mosanyengelela munthu koma kunena chilungamo.tamuikani nkhope yake pa Facebook kapena ma newspaper kuti timudziwe kutheka timakumana naye koma kamba kosamudziwa timangomudutsa

  12. Nzimu wa mlaliki wame umusake munthu ameneyu, nkhosa zosochera zambiri awame amayenera kuzilondoleza kwa atate kuzera mumaulaliki decemberyu. Mphambe achitepo kanthu.

  13. Apolice Athu Tisawanyoze.Chfukwa Murder Case Siyoenera Kuitenga Mwachbwanabwana Ai..Tieni Tikhale Pheee Afufuza Mpaka Munthuyo AMugwra..Tien Apolicewa Tiziwapatsa Mangolomera Osat Mphwayi..Tiziwafunira Kafukufuku Opambana..

  14. Dear Influential Individual, We are delighted that your life’s journey has led you to discover our organization. we value anonymity. We see and know all just as a shepherd sees and knows all of the flock, our eyes peering over the masses to identify any threat. We are the bringers of new dawns, the guardians of the human species. We are the Pyramid, the Eye, the Light, the Eternal. We are the ILLUMINATI. The ILLUMINATI is a collective of prominent figures throughout the world who have united to guard the human species from extinction,we create wealth and make our member famous and rich in their own line of work. Our members bear the burden of a planet’s leadership with the lives of 7 billion in their hands. As the human continues to rise above its other animal counterparts, governing of the planet has turned into a daunting task. In return for their loyalty, our ranking members are presented the opportunity for lives of limitless wealth and opportunity. Once a member, the requirements are unimposing and often spaced between many years. Our requests are simple and therefore may be hard to comprehend, but disloyalty is not tolerated. You must understand this before applying. Members must fulfill their oaths to the Illuminati under every circumstance and recognize that they are merely one part of a much larger Universal Design. For centuries, our organization has separated individuals of outstanding political, financial, or cultural influence from the flock, and established them as shepherds of the human species. Perhaps you have already proven yourself in these fields. For that, the Illuminati officially congratulates you. Your dedication gives hope to us for the future of the human species. If you would like to continue your application,and willing to pay a sacrifice start by reaching us on my facebook account JOHN FRIGHT and you will be added to our list of potential candidates for Illuminati membership,and you instant reward will be given you on the first meeting sincerely.

  15. God, lots of lives changed and follow you coz of this evangelist,we therefore ask your kindness n love towards him,take him to your place and leave wth him…he deserves to be with you.In JESUS name i pray.

    1. Osadanda kubwenzera ndi kwake kwa mulungu ndipo adziwe kuti omwe anamupha wame jahana ikumudikira ambiriii ndikukhulupilira kuti tinasintha ndi utumiki umeneu.We shall meet with wame beyond the curtain! !!!!!!

    2. True ccta koma zikundiwawa ine ndi mmodzi wa anthu omwe Evangelist Wame anandisintha kungomva ulaliki wao. I hv neva see hm bt hs voice and teachngz are stil alive withn me

    3. Simuchitanso kumufuna ameneyo, yekha akazipereka. Dziko limuchepera akanawerenge nkhani ya Kaini ndi Abel, sakanachitanso tchimo limeneli.

  16. Nanga bwanji anthu ena akutumiza ma video muma whatsapp a wanthu kuwonetsa kuti munthu wagwidwa, akumumenya anthu ndikumuphanso naye?

    1. Ndiye Thom chipinda akunena kuti we believe everything on social media, it’s our problem. Zina ndi zoti inu anthu nomwenu mukumatitumizira pa whatsapp. Nde ife titengepo chiti apa?

  17. Muntu akugwira ncito yamulungu, ndikuphedwa mosaziwika bwino, yesesani Apolice plz, Satanism yavuta kwambiri Ku Malawi pakalipano, Ana alakwilanji pokhesa mwazi waMuntu wamulungu????

  18. sicholetsedwa kut chokhumudwisa chisadze pa moyo wa muthu koma soka kwa iye wokwanilisa…. soka iwe yemwe walimbana ndi mtumiki wa Mulungu sunamalidze popedza tsiku lako likubwera Abusa athu tidzawaonaso lest in peace papa…

  19. Komatu asaone ngati amupeza wamoyo chifukwa ifenso tkusaka nawo kumupeza tkuyatsa basi,,,tzachita kujambula ka video kake tzakutumizraninso inu adm

Comments are closed.