A Mutharika agula galimoto ya mamiliyoni ambirimbiri pamene a Malawi akuvutika ndi njala ndi kugona mu m’dima

Advertisement
2016-lexus

Panthawi imene a Malawi ali pa mavuto a njala komanso kugona mu mdima, mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika azigulila okha galimoto yatsopano imene ikukwana ndalama zankhaninkhani.

2016-lexus
2016-lexus yopezeka pa intaneti.

Malingana ndi ma lipoti amene talandila a Malawi24, a Mutharika azigulila galimoto la mtundu wa Lexus limene likukwana ndalama zoposela K70 miliyoni.

A Mutharika anakwela galimotoli dzulo pamene amakhazikitsa ziphaso za mzika za dziko lino. A Mutharika anakwelanso galimotoli pa msonkhano wa chitukuko umene anachititsa pa Mchinji boma.

Galimoto la a Mutharika lagulidwa pamene a Malawi ena anadandaula kuti mkuluyi akuononga chuma cha boma ati pokhalitsa mu dziko la Amereka.

A Mutharika anakhala mu dziko la Amereka kwa mwezi watunthu atapita ku msonkhano wa mayiko a padziko lonse. Msonkhanowu unali wa sabata ziwili zokha koma a Mutharika anakomedwako mpaka mwezi.

Galimoto la a Mutharika layamba kale kudzetsa mpungwepungwe pakati pa a Malawi amene aliona.

A Felix Unyolo amene amakonda kulankhulapo pa nkhani zochitika m’dziko muno ati kugula galimoto pa nthawi ino pamene a Malawi akuvutika ndi kolakwika.

“A Mutharika akufunika mayendedwe a bwino koma osati pano pamene zinthu sizikuyenda. Uku ndi kuzikonda. Akanadikila kaye zinthu zizayende kuti iwo azagule gaalimoto limenelo,” anatelo a Unyolo.

 

Advertisement

810 Comments

  1. Bt he might put it in hz mind about de hard time dat malawians now are moving on bcz he himself can make plan about de action.

  2. We r different pple, he z de president. We hav to ask ourselves: Whose money ws dat? If de cash z his, congraturation Mr. President. Buy even a jet u r a president. Lucius Banda bought a hericopter but he z nt a president, car z cheap, too cheap.

  3. ngakhale atawina chakwera zithu sizingasithe coz ena mwaamene alibomawa akhoza kudzalowaso Mcp ndie kut lingasithe ndidzina lachipane kma atsongoleri sangasithe tien tisukusule amalawi muthu tisamamulore kusia chake chipan ndkulowa cholamura amasokoneza zithu ndiameo kmabe peter akadaganiza mofatsa ndi nzeru asanagure mgalimotori

  4. Poverty will kill you Malawi24 guys and fuck your dirty asses, Presdent is a high profile, you act as if you never went to school, being a Presdent it means he’s working and he suppose to get paid , why do you always find something to say whenever he does something? go to Mozambique poverty is there, go to Zimbabwe poverty is there too, go to Zambia troubles troubles, go to South Africa problems are there as well even in America you will find poor people what the hell is wrong with you guys leave him alone few days ago you made us believe that he’s dead now it’s a car, seriously? have you ever had anyone who was well educated in your family who would understand what does it mean to be working on a high profile or munangobadwa kumazalimbana ndi successful people?

  5. I saw the same vehicle that Apm bought in Limbe, # plate “KARIM 7 ” I was asking myself, if an individual can afford this car Wat more Mw govt? Enjoy Apm it’s ur tym

  6. MUkudan ndi ngalimoto bwanji? Muli ndichani inu or atakupatsani undindowo mungakwanitse, agalu inu osamalowetsa ndale pali ponxe mwanva inu amalawi obwera. Ndisavexo comment yonena President, unforded brain

  7. Apm sanabweretse njala,komanso alindi ufulu kugula chilichonse chakuntima kwake,akakhala magetsi sindiye akupangitsa kuzimazima amalawi talekani majerasi muzasitha liti khalidwe lotere zamanyazi

  8. Apm sanabweretse njala,komanso alindi ufulu kugula chilichonse chakuntima kwake,akakhala magetsi sindiye akupangitsa kuzimazima amalawi talekani majerasi muzasitha liti khalidwe lotere zamanyazi

  9. That’s Nyasaland don’t think these politicians care about poor Malawians ,Malawians r struggling to find food for their families but our politicians r busy squandering our money ,i feel sorry for my fellow Malawians

  10. Kuzolowera zolandira zaulele nthawi yoopsa yakwana. Budget amapanga ndi maMP OSATI President.umbuli bwanji mungoti kukamwa yasa kuyembekezera kulandira. Ine ndimadya zanga and I don’t wait for the President /Government to feed I &my family. Foolish people discuss people while the Wise ………………

  11. Its his money,Bravo Peter life is too short to enjoy,God bless you mr President, ndimasilira nditakhalako Puresidenti

  12. Zimakomela iyi Peter mntharika samamfuma kut tawamalawi tikhale pa bwino ndi chisilu Peter mnthalika ndikutha kwa ziko lapasi njala every year tizakhala pamutendele liti tigwile mutengo wanji a Malawi tili ndi vuto lalikulu mu dziko lathu.

  13. Kkkkk KO’d nsanje ilipobe et?akugona ndi njala chifukwa chaupoteleya and Ife tidakwatira timagona ndiakazi a2 osat njala and umana dollaryo akagulire zitumbuwa munthu openga wapanga bwa?

  14. Iwe sumagula nyama pamene abale ako kumudzi akudyera mtoliro? Iwe umafuna kuti poti kunjaku kuli njala ndiye kuti Peter adzigonaso ndi njala? Peter wagula chimanga chili ku ma Silos ku Kanengo, Nanga iwe pankhani ya njala wachitapo chani chimene dziko lingaloze? Kodi si inu nomwe munkati Peter wafa, ndiye lero wadzuka wagula galimoto yodula? Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkk

  15. izi zomati njala njala while you knw dat the problem was mvula bt u ar busy puttn a blame on bigman himself as if iyeyo ndi Minister of Rain in Malawi bwanj…………. ati magetsi magetsi, nde munamuona kt akuzimitsa magetsi? or nd News it analengeza zoti mtsogoleri wadziko lino wakaniza kuyatsa magetsii? ndianthu angat agula magalimoto odula while ali ndi azibale oti akugona ndinjala……galimoto nkukakhalaso ya boma……pamene yafika Malawi-pa or mtsogoleri atati agule drink #Frozy weni weniyu muyankhulaso ndithu……..kaya sindupanga nawo ine……

  16. Anyuzi paper muzilemba nkhani zomvekabwino mwasowa zolemba nonse ndizusiru za anthu ,vuto lanu ndi chani nthawi zinse mumafuna kupezelapo chifukwa pa nkhani iliyonse mbuzi za anthu

  17. Aaaaaaaaaa nanga a amalwi azabwere liti wozatitukula mmmmm abwere ndioyipa uyu ma mistake kma mwayiwala kuti munthu akachita chabwino muma yiwala koma akapanga mistake number 1 kukumbusa kma let de president enjoy him self mukuwona ngati kudandawula kwanu kubwezeresa zose nanu limbikirani chabe muzafike akulu anena kuti limbikirani xul mwano chocho umbuli nduumene ukutubwezeresa mbuyo coz woganiza akudya zake pheeee kkkkkkk

  18. Inu mumati agule chiphapha kankha ukwele komaali mtsogoleri wadziko?chikhakaso adatelo bwezi mukutiso chani pamene wina adagulitsa ndege uja ndalama zankhani nkhani mudangoti phee! Mpaka ndala zidamila zanu izo amabungwenu

  19. President Is One,not Two Or One And Half.No Mistake Is There,we R Different Ppo,different Mind, I Am Not A Dpp Member Komano Mukufuna Iye Atani?Azgawa Ndalama?Ndalez Muzsiye Kaye.Mai Aja Anagulisa Ndege Yathu Ndalama Siznaoneke,koma Big Akubwezelesa Ndiye Mut Walakwisa?Mabi

  20. President Is One,not Two Or One And Half.No Mistake Is There,we R Different Ppo,different Mind, I Am Not A Dpp Member Komano Mukufuna Iye Atani?Azgawa Ndalama?Ndalez Muzsiye Kaye.Mai Aja Anagulisa Ndege Yathu Ndalama Siznaoneke,koma Big Akubwezelesa Ndiye Mut Walakwisa?Mabi

  21. President isn’t to blame. After all, this issue was agreed in parliament and moreover ‘8’ were the cars agreed to be bought, so why blaming president for purchasing one car ? You mean money used on 1 car can solve all the problems we are facing ? You Malawi24

  22. b4 he bcom a president h was ored have money n every month he get paid wat z ur problem guys wake up mind ur own bznec even the can buy 100 of them I dnt care t z his tym I work hard nt to suffer neither to beg I dnt blame him I lv him so much u ppo from malawi u have problem any president u have a negatv attitude about him u want a president to gv u money wile u ddnt wrk ur vry stupid dear z no president hu can walk door to door bring u food never I lv peter Munthalika my president so stop tokg nonsense

  23. Kodi ndiye kuti munthu amakhala mtsogoleri wa dziko NDE kuti alive ufulu zalembedwa apazi nzopanda mutu and amalemba akuwonekeratu kuti anabanda chosauma

  24. Kuli mvuto kuno kwathu ku malawi anthu akamuona munthu atapanga chinthu cholozeka basi nkhani kukhala yaiye eeeee abale tiyeni tidzilimbikira tidzipanga zathu nafe munthu asagule njare?

  25. No matter that our country is facing problems I wish our president lives a poshy live style.
    This is what I expect from someone who failed to make it in the USA for good fourty years.

    I wish he builds a the best hospital within the perimeter of State House.
    I wish he buys an executive jet with all medical equipment fitted in.
    I wish he buys private life after this life full of lumbargo.
    I wish all these five years he concentrates on his wellbeing then consider Malawians if he gets into second term.
    I don’t care him having medical covers wealthy our national budget overseas
    It really doesn’t matter if he spends extravagantly to prolong his life until 2040.

    It matters if all Malawians will live happily without much problems.
    I like APM let him enjoy the best he can have this time.

  26. Ndipo bola akanagula ndege chifukwa a Malawife sifunilana wabwino kose dziko lathu ndilotchuka nditendele koma miseche ndikaduka ndiye osanena

  27. Apulezidenti Pita Tidawalemba Ntchito Ndife Amalawi And Amalandira Malipiro Awo Mwezi Uliwonse Ndalama Zimene Amalandira Akhoza Kugula Chilichonse Chimene Achifuna.Anthu Oyipa Inu Musade Pulezidenti Mavuto Amene Alimuno Malawi Pakufunika Tonse Ngati Amalawi Tigwirane Manja Tithese Vutoli.

  28. Chokani agalu inu mkuganiza kuti salary nya Profesor A siikukwana kugula galimoto?Ndalama zomwe wagulira galimoto zikanathesa mavuto anjala?Bwanji mwaiwala Muluzi anagula mabasi aYANUYANU SPECIAL mnangoti chete!Lero Mthalika wagula kagalimoto kamodzi zakuwawani.Phokotsa Chule silingalese Njovu kumwa madzi.SCHMO means= .

  29. Ngt agula galimoto yandalama zambili ndie achita bwino.kodi inu mwaiwala kt nthawi ya mkapen ija mumatiuza kt a peter ndi ndiolemela? ndie lelolo alakwitsa kuzigulira galomoto? aaah mwangofuna kt ifeyo tingoziwa basi,ndathokoza kut mwatiziwitsa.

  30. Kodi mtembo ugulanso galimoto bwanji? Amalawi timatsutsa zabwino ndizoyipa zomwe, madzi akuvuta,kodi mvula amagwetsa ndani? Magesi poyamba nyumba zinali zamagesi ndi zingati? Nanga pano ndizingati? Njala yayamba ulamulilo wa DPP wu?

  31. anthu yenawa ndiwopanda pompano anayakhura wokha ndipakamwa pawo kuti dzikorino ndirosawuka tiziti taremera kare zaka zomwezi tindarama tomweti tamisokhoti nditimene akuyimira pachulu kuti agula garimoto choti mudziwe chakuti mudziko muno muri wuphawi wambiri choti mudziwe nchakuti wotaya makoko sayiwara koma wakudya zithuzo

  32. Komandiye malawi 24 palibe chomwe wanena.kodi sadye nyama koma thawi yomweyo manong’onong’o asa tchene iwe zonena Zambilimbili.vutolako ndi chani?

  33. Amalawi kodi ndiliti limene tidasangalala ife? Koma galimotolo chikhala kuti ida gula nduna bwezi mukusangalala.tiyeni tidzukeni.mukufuna a gule galimoto lofana ndi terara? l

  34. kodi iye akugwira ntchito angalephere kugula zithu zapakhomo pake? u ar stupid so y he iz working? du u knw that to be a presdt iz also work like the way u work? masendeeee mxm

  35. “Chitsiru chimaika mtima wake kuphwando, koma wanzeru mtima wake ku nyumba ya chisoni.” Just quoting the bible, U canna argue.

  36. u people must know dat president amalandila salary yake mwezi ukatha so let him do wat ever he want with his ndalama mavuto anjala its not his problem people must lean to depend on your self not boma

  37. vote yanga atezatenge ndi manganya basi, man ofcos nthawi yabakili chimanga chimasowa koma ndalama yogulila timayipeza koma awa ndiye ziko lawakana bas mpaka chimanga k12,000 ife nde tikaba kuti ayambe kaya wasisa chimangacho then azigulabwino galimoto yakeyo haa koma ine ndiye wandikwana ngat kuvala malaya a 50cent.. manganya bwelamwachangu mwina ungasithe malawi

  38. ayi ayi musiyeni Amalawi umbuli mukulimbana ndi munthu mmalo molimbikira kuti nanu mukhale ngati iye,tapezani nkhani ina,inunso a news 24 mumaonjeza kya nanu muli gulu la mbulinso sindiziwa

  39. Wakeup!If acompany isnot selling does not mean people wont receive salaries,wont buy stationary and coffee.The office of president had this budget since DR Kamuzu was there.But,as time went things are getting expensive according to make and the like.Lets take it as ours,he is our leader,he deserves more than that.Lets work had because future leaders will need more than that where by will even have no adrop of water.My appeal to the MG IS TO MAKE SURE NO ONE IS GOING TO DIE WITH HUNGER BECAUSE many children has died in the hospital especially those born before 8months and we lost our twins this yr because of black out and the govt must be eyeing on that too.

  40. Koma musaiwale 1 to 2 years azakumbuka ndalamazo ndipo tili pa mavuto pa malawi sitizapezaso president wambino monga madala Dr h kamuzu banda panopa tili pa ulamulilo wa asamunda muwafuse asamunda monga amene akulamulira panopa ndi musamunda ameneyo bwanji sakufuna ku tukula analakwa chani mai nanga bakili panopa pamalalawi pavuta kwa zaka 6 akazachoka ameneyo tizaone chakwera mwina tingazapeze bwino mapeto a malawi boma lizakhala mmanja mwa amene ndi makomanda ngakhale pazavuta bola ndipo mlimazi inu mumazuza ana amasiye ndi olumala kwamulungu ndimoto ngati kuli oyamba kupeza mtendele ndife a malawi ife kwathu nkuvutika mapeto azonse ndi ulemelelo basi

  41. I don’t think Lexus 2016 is very expensive car for a President . I lived in Malawi for 7 years as a refugee I know how much life is hard but honestly Galimoto iyi siyodula kwambiri I drive myself Lexus 2014 so for President even to think of buying Lexus is a sign of care and love for his nation. This car is only $35,000.00 . Tisakwiyise mukulu uyu . President wa ku Burundi akuyendera galimoto ya $295,000.00.

  42. Kkkkkk Debrah Wa Naziyaya zoona zake ,mumati wafa kenako mukuti iyayi mkono wamanzere pano mukuti galimoto yatani ? Mmesa Ali pa ntchito nzanu asagule galimotooooo !!!!?????mukuti chani adaa

  43. What kind of afather,who does’nt care or listen to the cry of his own house,failing to buy akg of maize flour for just one meal,instead he goes out and buy an expensinve fone!!matama eti!,pali nzeru apa?anzanu akulira koma inu nkumaseka.

  44. Jacob Zuma spent K1.5b on personal house just mentanance.so what are you talking. Go to villages write stories of farming.children abuse it will make sense

  45. Malawians lets open our eyes please. Still sleeping until when? Moyo kungokhala odalila dzolandila siwabwino. Mwachita bwino apitala kuigula imeneyo

  46. ayenera kugula mesa naye amagwira ntchito mesa naye amalipilidwa akadyela kuti ndalama zake nayense ndi mnthu ngati ife tomwe kulikonse kuli mavuto tikayang’ana kwambiri kwa asogoleri tizakhala ovutika mpaka kalekale tiyeni tiphunzire kupanga zinthu patokha tisamadalire wina kuti atipangire anthu onsewa akugula zimagalimoto zopumawa ndikulimbikira kwawo osampangisa mnthu kuti akhale opempha pempha chifukwa cha ife ai Mulungu amadalisa opereka osati olandila nanga tikakhala olandila daily azatidalisa bwanji?

  47. Galimoto yo siyake ndi ya boma, just upgrade to be qualified for the presidential candidate for u to use that car in #2019.
    Jelousy bwanji madala!!

  48. Koma dziko la Malawi ndi nsanje silizatheka ndithu busy ndi za ziiiiii mmalo mopanga zanu Kodi inu munachepa nthawi ya muluzi njala inja simunaiwona mwanena zambiri pano za moyo wake ndipo ambiri mumafuna atafa si ntchito yanu ndi ya Mulungu kumutenga munthu,lero mwayambanso zina kkkkkkkk ndi inu omvesa chisoni kwambiri Kodi galimoto ziyendela ma president ngati imeneyi??,muzafa osauka ngati simusintha mtima wa nsanje mumafuna mpaka aziyendela njinga ya kapalasa (stop jealous Mulungu azakudalisani)

  49. Aaa vto ndi chan mesa imeneyo ndi ntchito dziko lanjal ndi lanjala. Munthu alephere kupanga zake chifukwa cha chipan kapena kulamul dziko. Aaa wauka kwa kufatu. Musamuletse kujoya moyo ngwaufupi uuu kkk

  50. Mavuto a ife amalawi ndi amenewa mukankhuta nsima zanu uko mukumalemba zopusa galimoto yomwe mukuinenayo ena ndiyopitila kumowa vuto lanu ndi chiyani •wamkachisi ayenela kudya mukachisi it never rain but it pours

  51. mukakhala ndi ndalam mumaonangat aliyese alinayo mukamadya m’makom mwanum musamaone ngat aliyese akudya oyankhula zabwin tuziw kt mwapana banzi kukamwa mukukanika kulankhula ovutikafe tizidyabe makoswe ndizitete odala ndinu amoy ife nde mwatipha tikudikila kubwela kwanu kut muzatimange ok all de bst

  52. Kodi muzingolemba zilizonse?inu mwagula mbaula,nyali,komanso trauser la jeans za new1 alipo wakulondani kapena kukulambani?leave this guy alone.

  53. Izidi Ndie mbweleladi munthu wagwila ntchito, ndalama ndiyako choiopela kugwilisa ntchito ndichani?????! Opusssa walemba nkhaniyi ayankhe!

  54. Mmmm! Mbale umutenge msogoleri kukhala bambo ako ndiye anthu aziwanena ungamve bwanji? Tiyeni timuremekeze msogoleri ngati kholo lathu….

  55. Ndalama wagula galimoto za boma.kudula ndalama Ku nduna za mamphunziro,zamoyo ndi ulimi mumafuna kuti mugule ndalamoto yamunthu imozi anthu anzivutika.Zopusa!!!! kodi amalawi muzakula liti? wadalembweredwa ntchito munthu yo ndiye wanchito wakukhala ngati bwana bwanji.

  56. koma zimene akupangazi sakumapanga munthawi yake munthuyu anali kunja posachedwapa waononga mitsonkho yathu yankhaninkhani panonso akugula galimoto,katundu mumashop wadula kwambiri.chimanga ku Admarc chadula bola kukagulaso kumavenda ndiye wina mkumanena kuti sanalakwe kugula galimoto ,mtsonkho ukakhala kuti ukulandila kasalale kabwinoko mtsonkho amakudulaso kwambiri ndiye anthufe tithandizikila kuti?

  57. Aa agula imodzi yokha? Amayenera kugula asanu asamafinyike a malawi mumayankhulitsa inu mumaona ngati kuyendetsa dziko ndikophweka….akuyenera kuzipepesa kumene pachipongwe mumayankhula chija

  58. Big up boss waine tikwele zimenezi munthu akamagwila ntchito zimafunika choncho kusiyana mukanamwela kapene kupasa MAHULE .

  59. kodi mumafuna kuti aziyendra galimoto zakutha inu mwasowa chokamba eti ….munati wamwalira panopa mukuti wagula galimoto ndiye!!! kulikonsetu magetsi amazima ,madzi amatha kusiya kutuluka komanso the whole africa is experiencing climate change and it is the global issue,,

  60. Mukuti axigulira okha galimoto inu mukafuna kt awagulire ndani poti ndalazo iwo alinazo zikuoneka ngati mutu wanu sumagwira bwino ntchito nsanje bwanji inu

  61. Malawi 24 Mulibe Nkhani Ina? Basi Mumvetse Anthu Mutu Mxieew!! Ndalama Imeneyi Ingakwane Kudyetsa Anthu Onse M’Malawi Muno?

  62. Too much jelous until when???…work hard and buy your own #passo or nissan note…size ikukana kumene…you think coz kuli njala ,,a president nawo azigona osadya?..kapena azigona mumdima?..nsanje siimanga mudzi pliz!!! Work xtra hard u willb promoted…..

  63. kodi kani sakulipidwa ? ndalama ndizamthumba make musiyeni asangalale alikugwila ntchitotu akuyenela kugula zofuna ndomunthu ngati iwe walembawe

  64. Zinateronso padzana paja, anagula magalimoto 6 odula kwambiri koma anangokwera kanthawi kochepa naye watsala pang’ono,, musadandaure a malawi, Mulungu si james amamva ndipo amaona!!! Ambuye Mulungu chitani momwe munachitira nthawi ijayo muchaka chogawika ndi 4 chinonso nchogawika ndi 4,, tikuzunzika!!!! Ameen

    1. Iwe Ndiwe Satana Wotheratu Ngati Zakuwawa Samuka Muno Ukafufuze Kokakhala Komaso Pita Tilinayenaye Mpakampaka Mavuto Awabweretsa Ndiyeyu Kunali Kamuzu,bakili,bingu &joice Banda Magetsi Njala Zonsezi Kulibe Iwe Ndiwe Bongwe Ulibe Njelu Nyanja Mazi Amabwelamo Mvula Ikwagwa Yambiri Ngati Mvula Inavuta Mazi Akawatenga Kuti Ngati Ifeyo Acompany Ya Illovo Mizimbe Yathu Ikuwuma Ikusowekera Madzi Ndiye Ndikamude Pulezident

    2. This really too much
      Hu ever is supportin this stupit president may ur souls rest n hell
      U dot know hw pple r suffering
      May God see us thru

    3. Ma cadet simunati mulira pompano ingotini pheeee!!! iweyo ukumubakirawe umalandira ndalama zingati ku Illovo? umathandiza anthu angati? ubwere udzakhale mtawuni mpomwe utadzauziwe moyo

    4. States yake iti iwe? kusauka kochita kukupanga? Anthunidi simmaona zinthu zomwe zili mdziko mwathu muno eti? mudziyenda mwamva, tili ndi madzi omwe amakhala chakachonse oti tikhonza kulima mbewu/chimanga mwakabwereza pachaka koma utsogoleri uli busy kuzikundikira ndi kuzitamandira, inu mkumaombera mmanja koma chikhalirenicho umagula kaufa kamujumbo daily!!! wake up malawians and think deep, osamangoombera mmanja zilizonse,,,, inute ngakhale mtsogoleri atakhala wakwathu ndimamuuza point blank!!!

  65. kkkkkkkkkkkkk spare my coment mungatukwanitse mafupa…sindikuonapo nkhani apa!!!… Access to information bill must be passed mwina muzilembako zamzeru…pali nkhani apa? Ndale ndi utolankhani tiyeni tisamaphatikize…for sure we are all politicians but lets see isues to politisise or not!!!…

  66. Sitikunena kuti kugula Galimoto mkolakwika ai,koma nthawi zina pofuna kuchita zinthu.monga bambo wapanyumba umaona Kaye mavuto aakulu amene uli nawo, sumangopanga zinthu mwa chimbulimbuli,Kuno Ku RSA mayor Wa Ku Pretoria ,atangosankhidwa. Boma linamugulira magalimoto apamwanba,koma iye anakana,m’malo mwake anaipereka kwa a police kuti aigwiritse ntchito,pofuna kuchepetsa hayi jaki mu mzindawo .Tsono ndiye pali anthu ena akungoombera m’manja koma milomo ili mbu kutuwa zachisoni amalawi anzanga .

  67. Kkkkkkk malawi wumphiwi wafikadi pachimaketi golimoto loti amagula munthu m’mozi mpakana kulalatachonchi, galimotolo ndilaboma 2019 mukazawina ndinu amene muzizayendela zanupheeee

  68. Nkhani yanjala sitsogoleri chifukwa winaaliyense alindimunda. Musadane ndi galimoto kambani nkhani ina kkkkkk general.

  69. Ndiye ??kkkk koma nkhani zinazi ! Kkkk I don’t understand, mumafuna agule ya 1million ngati yanu ?Let’s understand kuti president ndi VIP mumafuna adzifanana ndi inu? Kkkk limbikirani coz iyeyo analimbikira kuti afike pamene alipo.Musaiwale munthuyu ndi professor,olo asanakhale president amakhala moyo wofewa kuposa inu.Mxuuu zamkutu baxi mwasowa zolemba eti ?

  70. Chimene Chikundiwawa Nkhani Yachimanga Venda Akukulitsa 250 pa kg boma likutigulitsanso 250 pa kg ndiye pamenepa boma likutiganizila amphawife? chifukwa timalimba mitima kuti tizithawila mwa adimaki komaai nakonso kuli mpene,ndiye ndikudabwa anthu enanu mukumakhutitsidwa ulemelelo wa wina osayang’ana zaumphawi wanu mwatani kodi?

  71. I was thinking he buy bugatti or porch or Lamborghini I was about to say yes he is spoiling tax money for poor Malawian people that cheaper cars Daihatsu well done Malawi government.

  72. Mupite kumudzi mukaone n’mene anthu akuvutikira. mukamakhala town muno mukuganiza aliyese akudya kapena akugona nyumba yabwino. Sir Soja Lucius Chidampamba Banda adayimba zoona kuti tikamavutika padziko pano chabe zimangokhala nkhanza za anthu ena. So anthu ake ndi a ndalewa so koma tsiku likubwera chowuluka chidzatera!!!!!!!!!!

  73. Amalawi ife vuto ndi umphawi, palichiyani apo? Ndimayesa wagula ndi ndalama zake? Iye akugwila ntchito mwamva kuti watenga ndalama zaboma, tili ndi vuto lalikulu akalephele kugula chinthu chake kamba koti mwamupasa udindo zisilu, mbuzi za anthu.

  74. Iye zawumphawi akumvera kwa ife nde muti angatani presidentiyo?ankat musankhe ine wolemera cholinga anzazunze anthu.Bola mbuli Bakili adayetsetsako kusiyana nd Profesor hahahahaha

  75. Sizowona kugula galimoto lodula pamene a Malawi akuvutika.Kunali kwabwino kuchepetsako kuthimathima kwa magetsi omwe afika pokhumudwitsa zeedi.Kuvata kwa madzi a m’matapu,kulimbanako ndi njala mwa zina.

  76. Ha guys ndimaganiza kt bwanji tisamataye nthawi yothu mkulimbana ndi andalewa coz onse nchito zawo nzimozi olo akachoka awa o bwelalawonso mchimozimozi mwinanso adzakala wesi

  77. Akugwira ntchito nde mpaka asamatukuke malipiro awo onse azipeleka kwa anthu nde ntchito imeneyo iti iti? munthu uzachoka umbuli liti

  78. Mukamati njala mumati m’thalika aziyenda khomo ndi khomo kugawa nsima? Bwanji osaimbako mlandu anthu amene m’ma bin mwao mukumapezeka nsima kuti asamataye koma azikapasa anthu anjala.mbuzi imadya pamene ayimangilila msiyeni munthu nthawi ndiyake. Mukanakhals inu mukanatani. Nthawi ya kamuzu, muluzi, bingu,Joyce kunalibe njala samagula zinthu? Pangani zanu agalu amsanje inu.

  79. machende anu khani izingokhala imeneyo wakutumani chakwela eti takambani zina zamzelu kodi mesa ndi president eyeyo nde asagule galimoti

  80. Hahahaha bwanji osagula ya 2million, kuti nteleshe otsalawo tikonzere zinthu zina Malo moti aononge ndrama zonsezo mmmm zinazi kodi kumakhala kuopa kufa kapena chiani moti ka ipsum mabwanawa sangakwere? Koma moyowu mmmmmm kayaaaaaaaa

  81. politisize chilichonse bwanji zikugwilizana bwanji njala ndi kugula galimoto chimanga ku admarc kulibe? chasowa chimanga ku admarc? chikanakhala chimanga kuti kulibe bola

  82. Muluzi dd th dame whn h bought Bentry whts wrong wt you? H iz working nsanje basi, usova,iwe unagula bwanji plasma amalawi akuvutika ndi madzi osefukira mchilobwemu! Kkkkkk

  83. kodi kulibe anthu wamba akuyendera ma range lover udula abwerawa ama million? nde munene president azingoyenderabe za kale za nthawj

  84. kodi kulibe anthu wamba akuyendera ma range lover udula abwerawa ama million? nde munene president azingoyenderabe za kale za nthawj

  85. zinazi polemba muziganiza nthawi zina kumapanga manyazi zoona kugula galimoto yodula ncchifukwa ndipo ndinu anthu antunduwanji osafunila ziko lanu zinthu zabwino komaso even mutapita ku south africa mukapeza mwana wa school akuyendela the same car nde poti peter. wagula chikhale chifukwa shame Malawi ziko ndi anthu ake ose osalila, Ndikanakhala ine Mr president ndikanagula 10 osati imozi

  86. Choka iwe munthu oipa peter ndi munthu oputsa mdzika yoyamba ndi iye akanakhala wina bwedzi akuganidza za mavuto adziko osati pamene anthu akulira iye ndi kukagula galimoto ndiye mitsarayo kodi ndi minyama kapena walozedwa alaaaaaah

  87. Zakuwawani mene wagura galimoto km akanagura njinga nde bwezi mukuseka mt alibe nzeru ndekt mukumasowa zoremba?yambani kuphika zigumu anthu azikugurani

  88. Amalawife stizatheka bas mpaka kalekale coz timakonda ku hater presdent pa chilichonse chomwe angapange pa thaw yomwe ali m’boma komanso ali moyo kma akamwalila kapena kuchoka m’boma ndipamene ndye timayamba kumuyamikila pa tchto yomwe wakhala akugwira.Tinatan kod amalawife?kd tizasitha lit khalidwe lathu loipali?aaaaah nanu olemba nkhani bwanj mumakonda kulemba nkhani zot anthu azimpezera zifukwa presdent bwanj? Mukuyenera kusitha malembedwe anu ankhan osat zamilandu zanuzo nthaw zonse

  89. Mesa utsogoleri ndi ntchito ndipo amalipidwa,nde mmati malipiro akeo azitani nao(muli ndi vuto lalikulu musiyeni asangalale ndi nthawi yake ok,mind yours

  90. Chitsiru ndi bakiri muruzi kutenga dziko kupatsa chitsiru China vayachi akati chibungu chatizuza kokwana kenako kuvaya kubwera chitsiru chinaso chi joisi banda kuzidyaso ndarama athuso ndi nuzitsiru kuvoteraso chitsiruso chi pita panondiichi chikukuzuzanichi musova chitsiru chi bakiri muruzi

  91. Musiyeni president munasakha ndinu rerowaipa atase boraine ndi nakuthawirani Ku marawi kwanuko kwamaruziko azidyadi ndaramazo mesamukati ndi wagere rero gereija ndi imeneyo muziwona mwakura mwatha musova

  92. Anthu enanu ndinu wodwala.akati wadzigulira chikutanthauza chani?monga galu iwe ukunena zoti ukadagula yoposa pamenepo poti anthu akati adamwalira uli ndi zeru iwe mbuzi yeniyeni ngati boma sinapange plan kugula galimo iyeyo wangula ndikumati ndiya boma komaso ukuti anthu adzigwira ntchito ndikusapota mabanja ao ukutathauza akagwira ankhoza kuthana ndi vuto la esicom

  93. Ndimavoti anu musadandaule mudalakwitsa kale pa 19-MAY-2014 pompaja,tiyeni tidikire mu 2019 bola osazaphonya,chifukwa kulinso nthawi yawo ya kampeni imene adzakhala akukukondani pakali pano siinunso ofunikira iyayi

  94. Njala imabwera pa zifukwa zingapo,pena kusagwa bwino kwanvula pena kuguga kwa nthaka.Vuto ndi loti a Malawi timaona ngati njala imabwera ndi boma kapena atsogoleri.Mtsogoleri aliyense amafuna atasangalatsa munthu aliyense mu dziko lake.Zikamavuta atsogoleri amavutikanso m’mitima yawo.Ndi Mulungu yekha angathe kulamula Mokomera tonse a Malawi.Zinthu zavuta,zavuta basi tivomereze pano tiyenera kupeza njira zozithandizira.Kulibe mtsogoleri ngakhale m’modzi tonse tizamuyamikila.Kugula galimoto musakupange kukhala nkhani yoti wina aipe.Ndale zoipitsana zikungobwezera chitukuko pambuyo.

  95. Prophet Shepherd Bushiri already purchased 100 + million Kwacha Vehicle so how about President? lets just focus on other issues like how we can end the electricity deficiency. Mr President Purchase one for me, Just one Duet plz

  96. Galimoto imeneyo dzina lake ndi Lexus pa Joburg pompa akukwera ndi anthu a ma buziness ang’on ang’ono ndiye wht abt President wa dziko ngati dziko silikuyenda bwino pedzani njira zina zoyenera kuti mu yankhule naye,koma galimotoyo akuyenera kugula bax president asamacite kuyendera Toyota camry ati asove mavuto a dziko njeee man!

  97. God said ,’you’ll eat your sweat till death’.fight for yourself you’re born to fight.one man can not feed a nation,you’re just wasting time

  98. agula,ndindalama xawotu..and ur personal problems are urs..not his..ukakhala mphawi dont think that every one in malawi is poor..oky??!!!

  99. Ubwino ndiwoti olembato walemba kuti wazigulila, ndife vuto ndi chani? Chifukwa kuli njala ndikuvuta kwa magesi ndiye aziyenda pasi chosecho ali ndi ndalama zake? Mudeni pazina osati galimoto yoti wagula ndindalama zake.Dpp boma .

  100. Ubwino ndiwoti olembato walemba kuti wazigulila, ndife vuto ndi chani? Chifukwa kuli njala ndikuvuta kwa magesi ndiye aziyenda pasi chosecho ali ndi ndalama zake? Mudeni pazina osati galimoto yoti wagula ndindalama zake.Dpp boma .

  101. M’malo mothokoza kuti mulungu wamukondela ali ndi moyo.koma basi kumangochitabe zopusa .olo okukondelayo mkumakukondabe? mukachita chibwanatu abwana mulungu angokutengani,osadzivela chisoni bwanji? nsanje-chitipa mizimu ya anthu kumangolira!!!

  102. lol hahahahaa dziko langa how can president buy expensive car while we have more problems of our dziko (Malawi) apa dzikuchita kuonesa kuti muvi oyang’qnila suchedwa kulowa maso!! apa pofunika kupangapo khathu enough is enough

    1. Ndiombwambwana uyu musiyeni (empty tin) u president ndi ntchito wamba pali zambiri zomwe amayenera kukhala nazo a ngakhale asanalowe mu office. Ungomva kuti magalimoto umafuna kugulidwa anali 8. Kkkk. Amene aja ndi abwana mfana. Ndikuuze ngakhale lero itaonongeka bathing room ndi toilet zimawasatila zija ,mawa mmamawa! Chigalimoto chimene chija chikagulidwanso china chatsopano kuiwalanso kuti kwagulidwa Lexus. Chonde bwana President lero mukamapita Ku mulhakho mukwereko Lexus … Ungotaya nthawi

    2. ngakhale mundinyoze bola ndalakhula zinali kukhosi kwanga naneso ndi malawi ndiyenela kuikilapo comment ndili ndi ufulu inu ngat muli iziwa tsibwezi mukukhala black out mpaka 2days lol hahahahaa zanu izo mukazamaliza kuchemelera zopanda pake ndizaone kut muzapeza phindu lanji lol hahahaha yes bwana wake ameneyo ndichifukwa Malawi zinthu zizikulongosoka

    3. Galimoto yomwe mukudandaulayo ndi less than K80million. Tangofunsani magalimoto akuyendera ma directors mu ma company mu. Pitani pa Toyota (MW) mukafunse mtengo wa VX V8.. It is over K100 million. Go to Nissan (MW) ask for Nissan Luxury it is over K115 million. Lexus sikufikila magalimoto onse ndanenawa. Ngati munthu akutha kugula magalimoto amenewa. Kuli bwanji Gogo Chalo wathu yemwe china chilichonse akuyenera kupangiridwa. Yemwe a ngakhale kungotuluka Ku mpanda kuti angodusa ntauni aliyeeense kuima, chilichonse kuima. Angakhale UK ambassador.

  103. Mwalembazi ndi nkhani zopanda pake chifukwa ngakhale ndinakakhala ine ndinakagula ndege osatinso galimoto, ngati akukhala ndindege zingapo munthu m’modzi wa m’dzikomo ndiye bwanji president? kwa ine wachepesanso kwambiri

  104. Osamuikira Kumbuyo President Akulakwitsa Muzambiri Tnchito Yake Ndi Kukoza Mavuto A malawi Koma Apa Nde Wandinyasa Kwambiri

  105. Wats wrong do u want him to buy food en starte working at ESCOM? let him this is his era wait for urc,,,y cn’t u bring things he achieved stop fluttering things that bring no penny to pple tel pple to work hard in watever they du!!

  106. Nde iwe manganizo ako ndi otani osangopanga zako bwanji. Unamva zoti munthu wapenga ndi zimene iwe ukuchitazo wamva eti.

  107. umafuna aziyenda wapasi kapena agule njinga akhalae ngati iwe galu iwe opaanda nkathu nkomwe ufiti wakukulila iwe ngati muthu akungokhala akut chakudya amupasa ndi apulezindentiwo kusayenda ndikomwe kukupangisa ubwele kuno uzaone magalimoto odula kungwila tchito bas kupeza zosowa zako bas ndiye life. molo mot uzipanga zako maso ako pamenepo ukupanga za muthu oti zake zinayela kale ine ndisanabadwe nkomwe loi

  108. Vu2 lamalawi msanje yakula kd inu mungakwanise kudyesa aliyense payekha kd amalawi 24 . Kd mukufuna ife an2 osauka tisamalimbikile kuzidalira patokha kamba koti kuli boma mufuna an2 afe manja cifukwa codalira boma kd? Ngat inu muli anzelu pitani muzikalamulira mukayase magesiwo muthese njalayonso kd kucokela mthawh yasamunda ndicaka citi tinamva kt kumalawi njala yatha? Munene caka cake osamangobwebweta apa ai colinga an2 azikhala mwamantha kaya inu odalila boma kt lizikulimilani ine ai ndisiyeni ndizilimbikila komwe ndilinakoka.

  109. Muli ndi umboni woti galimotolodi wagula? Mwina mwaona ma cash sale agalimotolo eti? inu a 24 ine mmodzi wa malawi langa ndi pepho……… “UWONESENI mtundu wa amalawi ma CASH SALE omwe inu mwaona ngati umboni”

  110. Malawi sazatukuka chifukwa akuyendetsedwa ndi mbuzi. Boma loyendesedwa ndi alhomwe okhaokha silingalosoke. Anthu amenewa kukufunika akapange dziko lawo.

  111. About i my seif is not problem Peter Muthalika to purchase very expensive venicle becoz its the way to showing pple in Malawi his money you khow?so don’t waste your time to mock him.

  112. Beautiful answer from abdul …. That’s wt we call political quagmire & such sort of politicians never succeed at all …. Stop opposing unwisely ….

  113. Kupusa iwe ukulimbana ndi munthu Malo molimbika ntchito kugodomala uzikavuula mchenga Ku Nasolo uzikagulitsa Ku limbe kupusa

  114. Koma mukamalemba nkhani muzifotokoza momveka, mukamati muthalika wagula galimoto mukukhalangati ndi ya kunyumba kwake.

  115. I think a Malawi ndife onvetsa chisoni ndipo ngakhale Muthalika atulapansi udindo sitingatukukebe. Tikuyenera kuphunzira kuzindikira zinthu zofunukira kuzichita priorities. Muthalika payekha sangagule galimoto without consultations, ndipo anthu amene anamchita advise nde oipa chifukwa Iwo ndi amene sakudziwa mavuto a mdziko muno koma anasankha kuchita priorities galimotoyo instead of our problems

  116. Gays don’t worry pazimene achita apulezitemti athu pogura galimoto ya very expensive pamene amalawi akuvutika ndinjara,zimachitika ndizotha m’sanga.

  117. Simdimasapota chipan cha DPP ayi koma apapokha ndikomentako

    Kod koma mukudziwa kuti APM kukhala upulezidenti ndi ntchito ndipo naye amalipidwa? Nde mumafuna kuti malipilo ake asamagule zomwe iye akufuna chifukwa chakuti dziko lili ndi njala? Ahhhh muli ndi jealousy ndipo odzikondawo ndinuyo

    Akamadzagulanso magalimotowo atapuma udindo wake ndinunomwenso mudzidzamunenanso kuti wayamba kugwilitsa ntchito ndrama zomwe amkaba ali mtsogoleli

  118. dzana dzanali inu nomwe mudagundikatu, mumvekere akudwala akudwala,tsopano asadwale bwanji pomwe iye ndi munthu? amene samadwalatu ndi mulungu yekha basi, lero muli pa galimoto,musamaletu President is the head of the state,ali ndi mphamvu yotseka ka media kanuko

  119. Kodi ndkuti mukamangoti president wapanga ichi inu basi pa air kuchilengeza zikuthandizani ?? iyaa inu tawaunikireni aanthu zakufunika kolimbikira kuzigwilira okha tchito osati azichedwa ndizamkutuzi let the President do what is ryt..ngat wapanga cholakwika azapanga regreat ekha nthawi ikazamukwanira…thats y enafe tinangothawira ku Joni kuno tizivutika kuno inde koma tisamanve za anthu amabodza ngat a #news24….mxiew.ndatopa nanu kwabasi komaso ine zandale zanuzi sindipanga nawo..

  120. olamulila sakunganiza athu akuvutika kumalawi iye akungula ngalimoto yondula kubamdanzelu muntu wakulu osanganiza kunkhalangati mwana mwanaso alisondizelo

  121. Ndizomvetsa chisoni kwambiri kwa munthu wokhala ndi mzimu wa umunthu,anthu akugona ndi njala mmidzimu,tate wa anthu amenewo ovotawo nkumalakalaka mayendedwe ofewa pamene anthu ukuzunzika? Ayi sizilibwino,kukhala saatelo kumathokoza kumati zimatha mzako akakuchitira zabwino,kodi ndiye kuti amayenda wapansi asanagule imeneyi?

    1. Iwe martha,ine zoyambana ayi,ndakuuza kale,sinditha kukwiya ngati ukufuna kucheza ticheza bwino mmawa,ndikufuna ndizigona,iwenso usiku wabwino tiwonana,nanga ndatukana ngati?ankandikalipila kwathu ndili mwana ndikatukana,ndinazolowela mpaka pano sinditha kunyoza munthu,ukungondipatsa chimwemwe.

    2. mmene ukuonekela,martha ndiwe wooneka bwino,mumtima mwakonso mukhale mwachikondi koma nanga bwanji ukuoneka kuti anthu osauka ulibe nawo ntchito? samakumvesa chisoni? kapena umagwira m’boma ukuopa akuchosa? zambiri ndikuuza mmawa,ndatopa ndikagone usiku wabwino tionana.

    3. Amene mukusapota pitala nonse pachiphwisi panu ndikutitu palukundu panu. munthu wanzelu sangasekelele zimene zikuchitika mziko la Malawi ayi ndipo ndikupemphe kaja kadatenga bingu kabweletso nkuzamalizisa mtchonayi wanditopesa ine athu ovota azuzikilenji iyaaaaaa

  122. Atati asagule Galimotoyo sindiye kuti madzi abwera ocholuka mu shire river kuti a ESCOM apanga magetsi ochuluka ayi,ka ndalama komwe agulira galimoyo sikakugwirizana mpang’ono pomwe ndi dzindalama zomwe ayitanitsira chimanga kunja.A Malawi, a Malawi a Malawi-tatiyeni tikule pa ndale chonde.Ineyo mwina ndingoperekako maganizo anga.Chisankho chikachitika olamurira akadziwika komanso otsutsa akadziwika, pazikhala maphunziro apadera kwa anzathu otsutsa pa za matsutsidwe abwino.Kutsutsa komanga osati komasura kapena konyazitsa.

  123. Koma guys, ndege ena anagulisa akuyendera yobwereka mpaka galimotonso azikabwereka? Iya ngati ndi nsanje zanganyanya umphawi tikuchita kuukokomedza nchonchi bwanji? Mpaka wina asamwe tea chifukwa ndife amphawi kkkkkkk koma nyasaland

  124. xo whats ur problem inuxo ndamene mukusokoneza dzikoli galimotoy ndimene ingagwexe mvula kut magesi axamavute why alwayz mukumafuna kusokoneza mulimbane ndi akupaliament coz dis iz bil in new constitu

  125. M’malawi muno alipo mapwepwete amatha kugura 5 kamodzi nkamodzi abale awo akugona ndinjara. Apa mukukuwa coz 1 car? Kkkkk. Uphawi Ulichoncho anthu asiya kugura magalimoto?

    1. umphawi sizinthu nzanga iwe, #Victor vuto sii amalawife koma eni news paper kulemba mosinjilira nkhani mmalo molankhula zomveka bwino ku mtundu wa amalawi

  126. #Malawi24 njala mukuiona komanso mukuidziwa mmalo momachedwa ndi kulemba za lexus tagugulani chimanga mutigawile muonetse chitsanzo!

  127. Yes, He is entitled to becoz Malawi is not a poor country but our leaders are poor and wants to get rich hence they vay for expensive luxuries, KUMASYA UKAGU . UGALU UTHE.

  128. zinthu sizikuyenda bwino mdziko muno ndipo nkosayenela kutelo,pamene chuma cha dziko lino chikumka chikuweyetsekabe,anthu akuvutika kunjaku momvetsa chisoni tiziyankhula podziwa kuti Mulungu alipo,munthu ukanena maganizo ako sindiye kuti walakwa ayi.Palibe chifukwa choopsezela munthu kapena malawi 24 ayi,tikatelo timaonetsa kulephela chifukwa nkhaniyi ndiyoti yachitika.Maiko amzathu ukutukuka monga zambia,zimbabwe,mozambique,tanzania why not with us here? equals poor leadership from the grassroot level,we need to change for malawi to be transformed,leaders have an ability to change this country for betterness.

  129. Vuto lanu nchiyani?galimoto ndi la boma.Vuto lanjala si a president ai km climate change.APM akadya pizza wapalamula,akavala suit ya bwino waishosha,akaendaso wapansi wapalamula.MAPAZI ANU NONSE.

  130. i thought you would have saide he bought a presidential jet but a car ndiye mkumadandaula aaaa Malawian kukonda kulira always ayikhona

  131. Ndipo achita bwino! President ndi munthu olemekezeka kwambiri akungoyenera kumayendera galimoto ngati imeneyi….mmafuna aziyenda pansi or pangolo?? Ndipo agula si a President koma boma!

  132. odya zake alibe mlandu,iyeyo2 amalandira ndipo olo atagula ndege mlandu alibe,ee wamwalira ee nkono wamanja,ee wagula galimoto koma amalaw tili ndivuto mmh anakulakwiran chan a Muthalika?inu amakulondan mndan?koma munthu wina apanikizike cifukwa ca inu?mmalo moganiza maplan othesa mavuto panyumba panu busy kulimbana ndi munthu oti zake mzoenda kale mukuchedwa

  133. hahahahaha ndikuseka chabe mwati agula galimoto nde nd bwino agule ndegetu kut zikuwaweni kwambri inu #malawi24 kod #APM NDI AMBUYE YESU ETI KUUKA KWAOKUFA EEEE #APM ND KAWAWA ….2019 #DPP NDI BOMAAAAAAAA!!!!!!

  134. Let the president enjoy his time!!!!Big up mr president VIVA MRMUTHALIKA and down with jealous and envy pipo like panga zako tomorrow someone to admire you

  135. Mukati Anthu Akuvutika Ndi Njala Ndi Kugona Mu Mdima Mukutanthauza Kut Nza Chilendo Kwa Inu? Kapena Vuto Lot Wagula Chinthu Chodula? Inuo Mumangomva Zothaitha Za Galimotozo Adasainila Kalekale Ndie Yafika Nthaw Yot Agule Asagule Akut Pot Kuli Njala Ndi Blackout? Walemba Nkhaniwe Tandiuze Udagonako Ndi Njala Iwe? Mavuto Ndi Akale Awa Ndipo President Sadzasiya Kupangilidwa Zinthu Becoz Kuli Njala Ai? Ma Gelas Bwanji? Njala Ndi Ma Blackout Loadsheding Sizidayambe Lero Inu A Malawi20004

  136. Mukati Anthu Akuvutika Ndi Njala Ndi Kugona Mu Mdima Mukutanthauza Kut Nza Chilendo Kwa Inu? Kapena Vuto Lot Wagula Chinthu Chodula? Inuo Mumangomva Zothaitha Za Galimotozo Adasainila Kalekale Ndie Yafika Nthaw Yot Agule Asagule Akut Pot Kuli Njala Ndi Blackout? Walemba Nkhaniwe Tandiuze Udagonako Ndi Njala Iwe? Mavuto Ndi Akale Awa Ndipo President Sadzasiya Kupangilidwa Zinthu Becoz Kuli Njala Ai? Ma Gelas Bwanji? Njala Ndi Ma Blackout Loadsheding Sizidayambe Lero Inu A Malawi20004

  137. Uuuuuh man let him suppose it was you being the president would speak or talk the way you are !!!!men first point and think about yourself before talking and how many presidents have killed and did shit and bad things to their people but we continue voting for them why????in need of someone to eat our money while seated in term of ruling the masses(country)so even if you with your tears or blood its nothing men just let it be

  138. I never see any probrem on that ,meaning kukhara mtsogoreri uzi rephera Ku panga chinthu mmmm you guyz b4 post ur story think 1st I never see any probrem on that ,meaning kukhara mtsogoreri uzi rephera Ku panga chinthu mmmm you guyz b4 post ur story think 1st

  139. Kkkkkk ndechambacho munthu akadwala nthawi yaitali olo nzeru zimatha ngakhale alibe ndinkale, wanadwala chifukwa chofuna kuba ndalamazo, that’s stupid of him nkhoswe wachabechabe

  140. Kaduka komaso kusayenda mayiko anzathu mzimene zakula a Malawi. Galimoti limeneri ladulapo chani? Galimoto loyendela anthu wamba ngati iyi. Moti mpakana a president aziyenda wapansi ati poti kulinjala???.. Moti kuti tiyende malo ogulidira magalimoti sitikawapeza amalawi ena akugula magalimoto? Mmmmmm!!!!!.. Ndale zakufikani pakhosi, zikuphanitu.

  141. Lucias azigula denge koma ndi AP nde wat more president za ziiiu ndi tym yake nayenso Ali ndi ma plain ake opezela ndalama

  142. Anthu Ambili Panopa Akudzala Milazi (chimanga) Ndiye Winawe Ukudalila Kuti Apresident Amagawa Chimanga Chaka Chino Simuchiona Gwilani Ntchito Kuti Muzizidalila Ukangoti Manja Lende M.bale Uzingoda Aprezdent.Ife Anthu Akumudzi Timadziwa Vuto Siti Ganizakoso Zoti Tili Nd President,

  143. Should Mutharika come feed us in our homes? Our problems is that we are used to receiving food for free.We always wait for WFP,World Vision or ADRA Malawi to give us food for mahala.Whether APM buys expensive car or not its for him not for us to complain.Lets just keep working hard bcz complaints won’t bring bread on our table

  144. Vito ndi nchani? ndiposo wachepesa bwanji timakhala ndimoyo oyipa amalawi sindimukonda koma palibe nvuto pamenepo ndi mukufuna aziyendela zakale si bhooo amalawi

  145. Kugula Kwa Galimoto Kusabwele Chitonzo Kwa Prezdent Nkhani Imene Mukukamba Yanjala Ikukhudza Wina Aliyese Mmalawi muno Kod Mukuganiza Kuti Oroko Akadagula Chmanga Akadagawila Anthu Angati Zinazi Musamanyanye Ngati Kulibwino Muyimileko Inuyo Muzikatigawila Chimangcho Ngati Mukakwanitse,

  146. munthuyu sikuti ndiwolakwa, koma ngakhale anthu osalakwa sikuti Mulungu amawaikira malire amadalitso et, amankera kuwadalitsa malingana ndintchito zawo,,, iyeyu mukumut afa pita munthu wantalika ngakhale kugula imodzi galimoto palibe vuto ndalama xotsalaxo nkuthandiza anthu ena omwe tikuvutkafe znakakhala bwino ndipo palibe munthu amene anakamadandaulapakuchita choncho madalitso bwezi atagwetsedwa pamadalitso anzake, WHY? the more worries people have on your doings the greater the subtraction of blessing and this is not always verified by the way one loses his or her belongings and the vise versa.

  147. Choti Mudzwe Munthu Sayamba Uchotsa Chitsotso Chili Mmaso Mwamzake Chake Chili Mmaso Apresident Ayang’ana Kaye Vutolawo Komaso Inu Anthu Akutawun Mmayelekedwa Ife Kuno Kumudzi Timaunikila Timakoloboyi Koma Inu Magetsi Akangozima Pang’ono Basi Mwapezakhani Kwa Prezdent Kod Prezdent, Used Job To Escom Ngati Town Yakukanikanan Bwela Nkoni–

  148. amene wachta post iyi nd opepela coz u dont follow up matters coz that’s development ndye zopepela osamapanga pano ayi

  149. Samamva uyu.Timango vutika nkudzudzula basi.Momwe njala yavutilamu?moti kugwa kwa kwachakusakuona?Koma mmutumo zikuyenda?Msamatipatse zoyankhula amalawife mwamva? Bambo sangagule ngolo mnyumba mulibe olo wokomani ya ufa akatelo ndiye kuti sakonda banja lake.

  150. Pa Malawi njala ndi mavuto ena sazatha. Mulekeni munthu adzipepetse nayenso amve kukoma masiku a ku mapeto a moyo wake. Ngakhaletu munthu ukhale wosauka komabe nthawi zina umatha kugula ka 1kg ka nyama yambuzi nkudzipepetsa. Anthu inu nsanje bwanji? Tinene kuti akadzachoka m’boma omwe azabwerewo galimotoyo adzayikana kuyigwiritsa ntchito?

  151. Aliyense azadya thukuta lake. Mukuyembekeza a president akugukireni chskudya makomo mwanumo? Wake up Malawians,we don’t. vote president kut azitithandiza mavuto a pa khomo. Njala ili kulikonse,ask South Africans.

    1. Sammy anthu akumalawi ndi aulesi samafuna kugwira ntchito, ndiye ulesi umabweretsa nsanje. Timaiwala kt mulungu anamuuziratu Adam kt azigwira ntchito molimbika chifukwa azadya thukuta lake

    2. Zoonadi,pena pake timalankhula mosaganiza. Yes,I know kuli njala koma vuto lidali mvula. Si Ku Malawi kokha. Nsanje that’s why dziko lathu silikutukuka.

  152. A malawi24 first munakayamba kupanga criticize otsutsa coz I remember they are the ones who Accepted the idea in the parliament. Coz the reader of opposition s car was bought while the economic was in mess.

  153. Lexus its not expensive car that makes pipo to follow him because of that car ,pipo are full of shitt let him to buy any car he want on his self “meaning” he is president and he can do whatever he want, don’t forget that you pipo are the one who spreading feq death for him so now you complain that he bought expensive car kkkkkkkkkkkkk Bingu was the one who bought expensive car because I remember it was S400 benz not this one kkkkkkkk let him to enjoying new car lexus *died man

  154. .Are you good in bed ?Do you really need a rich sexy sugar mummy or sugar daddy that can change your life completely with money and influence, so get the opportunity to meet sugar mummies from all works of life,politician,bankers,oil ladies,executives,directors,gold ladies,cash money ladies,Global Network group friends,doctors, ladies, willing to pay as much and get the best exclusive VIP arrangement anywhere in Nigeria,LAGOS,ABUJA,CALABAR,DELTA,ANAMBRA,PORTHARCOURT,,RIVERS,KOGI,KADUNA,JOS,ABIA,KANO,BAUCHI, SOKOTO,BAYELSA,ONDO,OSUN,OGUN,BENIN,IBADAN,ONDO,BENIN, call admin on 09036713792 08117333727 for your connection,like page before calling.

  155. Ndizovesa chisoni tikuvutika azanu muno mumayiko ayena ngati ndalama zipo basi asogoleli athu thandizaninso mutundu wanu ndife achisoni

  156. Mukasosowa Zolemba muzingokhala kwanuko musamatibowe ndi nsanje yanuyo mumafuna munthu azitani? Wina ali ňdi ndege 20 mukuti munthu wamulungu, president azichita kuyendela lole kuntako mbe
    Zomwalila zija basi zatha mwayamba nkhani ina

  157. Dziko lamalawi panopa lilipachisauso chachikulu makamaka njala ndiye wankulu wachoka kukasaka amuthandiza baas ndikuponya nthumba mwache zovuta kwambiiiií liiiiiiiiii

  158. Or atagula ten sizaboma basis… Joyce sanazisiye?? Or pitala azazisiyanso… Mmaganiza mopepela bwanji?? Or asegule nde umphawi utha?? Amthu openga mwapanga bwanji??

  159. kodi mmesa department iliyonse imakhala ndi budget yawo yokwanira?zikhuzana bwanji ndi presdent kugula galimoto?????? Amalawinso pena zinazi ngati sitidziwa kulibwino kungoseka pakamwa,za blackout sizingakhuze presdent

  160. anthu mumafuna kuti fumu yadziko yiziyenda pagalimoto zokankha kawondo kawondo ? nanji ndi nifumu wosatukwana anthu anthu amene anali wotukwana ndi awa
    baki
    amayi aaaaa

  161. Ya wachita bwino coz akugwira ntchito nd he had already more money b4 he come presdent nkhani ya njala even nthawi ya kamuzu inaliko anthu ankalandila chimanga cha yellow kuchokera ku kenya even during muluzi term ppl were suffer 4 hunger if u can remember 2001

  162. Let’s talk what will help malawi buying a vehicle is not a crime did you find out whether the funds belongs to government I don’t think so remember he is on payroll he was working before becoming a president.woh

  163. Whats wrong with u Malawians? Owez complaining, if u failing to feed a family of 3 wat about him who taking care of the whole nation? Wat kind of president do u want then. He must come with food to ur houses? Does he control rain? Disgraced pipo

  164. Tili pa ulendo abale. Azanga tisadikile kuti boma. Lingatithandize zomwe zikuchitikazi. Sizinayambe reloo. Its about work hard.or dae witch njala sankha wekha

  165. Amalawi 24 inu ndemenr mukulowetsa ndale ngati mukudana naye pres. Peter kubwela poyera bwana ife amalwi 24 sikufunani not kumalemba mikuluwiko apa.koma tsiku ndilimodzi tidzamva kuti wina wasowa ku company yanuyo ndi manyi anuwa mumalemba apawa ndithu

  166. Amalawi Takondwanaye Kwabas And Akanagula Ziwili Ina Getrude,,,ndemkutiuzaife Mkuonangat Zatiipila? Ayende Masiku Omwewa Awa Pa Campain Tigulaso Ina Zitsilu Inu Et Osalembako Zanzelu Bwanj APM 2019 Akunyenyaniso Tinakadya Ndalamazi Ogona Mmdima Zanuizo Wavanjala Azingopita Ku Admarc

  167. Toyota Lexus is nothing people this shows that u just nothing but cheap people who just write nonsense here find something else to do that can help you to make money so that u can buy yourself a Lamborghini forsake leave the president alone shit

  168. ngati kuli media yo mbwambwana ndiye imeneyi #Malawi_24,ndikumphunzitseni lero,ndiye mukamaliza kuphunzilako muyitseke nyumba yanuyi sametime, OK! president imene ija ndi ntchito monga ukugwilira iwe watumiza nonsense zi,amalandila ndalama, amalandilanso ma allowance monga aliyense yomwe akugwira ntchito,ndiye zili ndi iye kugwiritsa ntchito ndalama zake kupangila kapena kugulira chilichose chomwe iye wafuna coz ndi thukuta lake,olo inuyo a news muthanso kutengapo mbali pa mavuto omwe ali mdziko lanu,learn to blame the government not the president pa mavuto ena ochitika mdziko lanu, …….

  169. Malawi muli ndi vat o kodi munthu akhala msogoleli akathetse njala kwanu asagule chithu chabwino abale ndichani a malawi

  170. whats the problen with buying acar ,buy ajet so that ucan fly.These pplo they r up to something.U pplo uwant your president to stuck on the raod

  171. Vuto la amalawi munangozolowera zopasidwa zogwila ntchito imakhala nthano kwaiwo chomwe mungadziwe sitili munthawi ya*#abakili ayi yomwe amagawe wayenera pano zinthu zinasintha tikumapita kusogolo zinthuso nazo zikusintha zikufunika amalawinso mudzuke ndikupenyesesa,osamango posta nkhani zopanda mitu ngati izi ayi changamukani amalawi

  172. Kkkkkkkkkkkkkk,azolowela kupanga zintu mwoputsaaaaa…..angomwalila basiii titsiwe kuti dziko latu ndilopanda President…. Aaaaaah tatopaaaa ifeeeee

  173. Vuto ala ife amalawi timayangana zolakwikwa za president takumbukilani bingu atagula magalimoto antundu wa hummer anthu anakamba zambiri koma magalimoto wo anali aboma Joyce naye anawagwilisa ntchito iyonse ndi yaboma siyake ayi akazasiya udindo enaso azaigwilisa ndye ntchito basi

  174. Well done mr president, now try to buy presidential jet, coz we are wasting lots of money for hiring these jets. Til today i don’t understand what JB did for selling that jet.

  175. Vito ndiumphawi kwathu kuno,sindiuona cholakwika pogula galimoto

  176. Amalawi ndinu atha osaziwa mulungu ndichifukwa uphawi uli nafe kakaka malawi hav lake yabwino,mulanje mountain yabwino miyala yodula yabwino kma stil tikukanika kulemera cox ndinu anthu okonda zachikuda xamakhwala so mufuna mulungu akulemereseni en chomwe ndingakuuzeni choti olo mutakhala kut malawi ali pa uphawi sizizatheka president kuvutika nawo en blame yo mps not chilichonse president mbuli za anthu amalawi mulikutali ndikulemera ambiri mukhalira kunyoza boma mpaka kalekale and muzafa aphawi amalawi ambiri cox simuziwa mulungu anyani nonse mukucommenter zopusa osaika pa mpando a bambo anu bwanj mutharika wangogura galimoto kma bsi muyakhule mukuiwala kuti mai anakuberan ndalama inu muli malawi momuno munapangapo chan

  177. ngakhale kamuzu banda amatelotso even bakili muluzu amapanga chimozimozi ndiye itsakhale khani coz wachita ndimuthalika. ntsiyeni ndalamazo ndizake amagwilira ntchito lnutso mutafuna mutha kugula bola ngati mukugwila tchito ok

  178. Nde mukutiuza ife kut titani? Timadya zanthu sitidalira za munthu mwanva. Timayamika mulungu potipasa manja ndi nzelu osati zopusa zolimbana ndi munthu.

  179. Ine sindikuonapo cholakwika coz mwezi ukatha amalandila,,,kodi inuyo mukagula chinthu amakhala nanu buzy ndi ndani kukufufuzani???? Tisayiwale kut wa mkachisi amadya za mkachisi

  180. So what? Mesa amalandila salary? mukufuna akugulireni chimanga ndi salary yakeyo? foolish criticism and argumentation. He’s gat rights to utilise his pay anyhow. mumatiimilira mr president…….i salute you

  181. Amalawi sadzatheka anadzolowela kupemphetsa,umasikin unaalowa mmagazi. Mudzayankhula mpaka lit? Musiyen adyelele sanalakwitse

  182. Inenso ndapanga kafukufuku ndapeza kuti dziko lotchedwa malawi ndi nambala one pa dziko lonse lapansi kaduka (jealous) mukufananitsa boma ndi 104 million kodi kugula chimanga kapena mankhwala anchipatala akhala angati kodi kwina kulikonse sikuli ndondomeko yake yogulira zinthu kodi speaker ndi opposition leader anagula magalimoto a ndalama zingati ya president yatchuka chotani

  183. Nde enanu ndikumaombera manja bwampini odzikonda osaganizira athu ake ngati ameneyo, manyazi alibe ndithu mene mtundu wa Malawi ukuvutikira, nde winawe uvekere peter yemweyo UCHITSILU BASI.

  184. Akuyenera kutero coz 2019 he w’ll not win nde akuyenera kupangiratu his wealthy, dats why he is busy kukweza mitengo ya zithu mukuziwa kale, ku maneb, ku ma colleges and now chimanga and lets wait more is coming, plz my holy God serve dis poor pipo in dis hand of evil leaders in de mighty name of Jesus na holy spirit.

  185. Nayenso kukagula galimoto,, nde bola akanagula ndege. Tzisiyanako nd president enafe, zoona ine kuyendera galimoto APM kumayenderanso galimoto,, aaaaaaah gulan #ndege abwana

  186. it’s that Village Malawian that suffers coz if these decisions, i mean those people that vote not because the one they r voting for is from their home village but becouse they believe that he or she will put them first, putting their taxes to the benefit of the taxpayers… laundry soap and water, the necessities to every being is being taxed… was the tax money aimed at buying luxurious vehichles while the tax payer is starving? no wonder ppo evade tax….

    1. What nonsense are you talking here? Wait for 2019 and remove him through the ballot if you can. You expected the president to be using Toyota Noah? He deserves all the comfort and respect.

    2. What nonsense are you talking here? Wait for 2019 and remove him through the ballot if you can. You expected the president to be using Toyota Noah? He deserves all the comfort and respect.

    3. sorry i responded the way u want, koma ine point ndiyokuti anthu akuvutika kunjaku… u and i dont need the president, ena survival yawo ndiyovuta without him….

    4. sorry to u too Martha Sinkhonde if i have offended you, my point still stands kuti anthu akuvutika kunjaku and they look up to the president, u and i dont need him coz we can feed ourselves… what i do for others only God knows if its enough, but a good leader puts his ppo first, just like good perents forcuss on their children… if u talk of deliverance, ambuye akhululukedi ngati kuwaganizila anthu osawuka liri tchimo

    5. The fact is that this so called pitala bwampini he didn’t win the election, he just stole the votes in conjunction with mbendela that’s why God Is punishing these guys by starting with mbendela and then it will be pitala little by little. What he want for pitala is for him to suffer first, he must feell the pain that’s why he will be back in hospital soon just wait and see

    6. kkkkkk eti Simeon, kukula konse kuja bwampini ameneyu azikhalira kugula ma luxurious vehicles mmalo moti azilapa machimo, size imeneyi moyo umakhala ukuthatu…afuna azunze anthu osalakwa asanafe uyu…

    7. Inu kwanu kulibe manda munameza miyala simufa muli bho a Nyirenda kutsogoza anzanu kumanda but know God is wonderful and can’t think like U He created everything for a purpose and Gods time is the Best. Today is him kudwala mawa its U and mi who knows censor your words Mr Idiot

  187. Ngati mumaona ngati bwampini anakhalira pampando kuthandiza dzikoli ndiye muchedwa nazo, he came for the luxury of it. Keep voting them to fund their ego

  188. Being a President he is supposed to enjoy anyhow because all the powers were given to him so dont put blame on whatever he is doing.why are you mummuring foolish things hence your parliament has approved it? a malawi tiyeni tizizidalira tokha tisamangodalira president chirichonse,kodi mamillion wagulira galimotoyo angathetsere mavuto onsewawa?a malawi siyani mtima womamulonda president.

  189. Iwe ukudandaula kugula kwa galimoto apulezident wasowa chonena umati alenzident aziyenda wapansi?mind ur busines and buy yours osai kuchedwa ndikuona zomwe ena akuchita pulezident simunthu wamba ayi!

  190. KODI GALIMOTOYO AKADAKHALA KUTI AGULA NDI AGOGO ANU,MUKADALANKHULAPO CHANI?TIENI A MALAWI TISIE SANJE TILIMEKEZE MTSOGOLELI WATHU .

  191. Chimena Amalawi tikudaula ndichikut abwanawa akhala kunja 1mth akhala akuononga ndalama zakhan khan sapanathe mawik awili angula galimoto landama zakhanikhan pamenepa aonjeza.ndasikimiza za bauble/quran kut masiku osiliza anthu azakhala ozikonda okha.poti mavuto apaziko lapisi siatha tien tingalimbikila kupephela tikakhale mmoyo wachimwemwe ndi chisangalalo kumwamba.

  192. Mafuna agule ngolo zoona ndi ma jelasi anuwo pali munthu anayamba wathetsa njala kapena president ndiamene ali ndi mvula pena pake amalawife tidzisiyanitsa president ndi munthu wamba. Ubwino wake ndi aboma not amunthu

  193. Kodi galimotoyi mesa ndiya boma? Atati aturuka m’boma a DPP 2019 (though I know DPP will still win) a MCP nkukhala olamulira mesa a Chakwera ndie kuti azidzagwiritsa ntchito same fleet of vehicles. Galimotoyi ndiya boma, why the noise? Tizingotsutsa chilichonse?? If there was a need for a new Presidential vehicle mmafuna akagule chani? Toyota Vitz??

    1. Ukufana unduuze kut vulo lomwe analiona pitali m’dziko muno ndi la galimoto yodulai????? Zot kuli mavuto a njala ndi magesi amenewa simavuto??? Kugula galimoto sikulakwa koma kulakwa kugula pa thawi ya mavuto ngat ino..

    2. So you want me to understand that akanapanda kugula galimotoyi magetsi akanasiya kuzimazima? Ndie kuti mmene boma lagula galimotoyi magetsi azizimano kwambiri eti??? #Jazili

    3. a oster ndinu okanika, nzanuyu akutanthauza kut; ndalama zomwe wagulira galimoto anakathandzilako kuchepetsa mavuto ena, ndikufunse paanthu omwe akuvutka mmalawi muno ndndani yemwe wathandzka pakugulidwa kwa galimoto currently,,, another thing is kuyendera galimoto yotchpa does not mean the user also is cheap no, he would still be honoured you see.

    4. Wagula ndi ndalama za boma ndipo galimotoyo ndiyaboma, nsanje ndiyo yakula apa. Kuvuta kwa magetsi ndi chifukwa chakuchepa kwa madzi mu Shire. Mumawoneka ngati ndinu anthu a chisoni koma ndinu mfiti ngakhale a neba anu simunawapatseko ngakhale deya. APM boma.

    5. Kkkkk kodi kumsonkhano kumene anapita bwampiniyo chanzeru chimene wabwela nacho ndi galimoto basi? Kuononga msonkho wa amalawi nkukapemphako galimoto basi. Zikanakhala bwino akanazimilatu nkulu ameneyi. Kodi kumalawiko mfiti zonsezo zikumatchukazo basi nkulephela kuloza nkuluyi aaaaaaa

    6. Nde mwat magetsi akuthimathima coz maz achepe mu shire ok tamva, nanga tiuzeninso chimene chikupangisa kut mdziko muno mukhale njala…

    7. mvula amagwetsa ndi mulungu osati president man ngsti mvula sinagwe ndiye mungalibane ndi a ppresident kagwile ntchito man kuti upeze kwacha kuzolowera zawulele et mwandi topesano

  194. Yambani mwatenga half yasalary yanu muthandize osowa kuti titsimikize kuti u rly heart the needy anthu otsogoza ndale inu. All u do is pretend u feel for the needy!!!
    Everyone must change! It begins with u.

    1. did he use his personal money or our taxes palibe cholakwika kufusa coz ifeyo ndiamene timapanga fund zinthu ngati zimenezi we pay tax

  195. Ubwino wake sikuti iyeyo amayenda khomo ndi khomo kugawa chakudya ai, aliyense amazipezera yekha chakudya chake. Ndiye palibe ndikuona chachilendo, wachepetsanso kugula imodzi. Titengerepo phunziro, tileke kugulitsa chimanga chathu chimene takolora tikatelo mavuto ngati amenewa azitidutsa. Ngakhale kuti, atagula jet yodula kwambiri sizizatikhuza chifukwa tizakhala tikumakhuta kwambiri m’makomo mwathu.

  196. Itayeni nkhani imeneyo ameneyo ndi munthu chimodzimodzi wina aliyense akhoza kupanga kanthu kena kalikonse monga wina angapangile.Mavutowa ngobadwa nawo palibe Chaka chomwe mmalawi simunakhalepo njala kapena kuzimazima kwamagetsi.President ndi munthu chimodzimodzi wina aliyense amasilira ndiye ngati wasilira kanthu asagule popeza ndi President, amalipidwa Ali ndi mabusness ake akhoza kugula galimoto. Moti mmalawi muno amene ali ndi galimoto lodula ndi peter yekha basi? Komaso inu apeter mwawonjeza zinthu sizimakkala choncho azanu ku South Africa azuma anabweza nazo ndalama Ku parliament chifukwa chake ngati chimenechi.

  197. Vuto LA amalawi timangoyangana vuto imodzi, tiyeni tiphunxire kuzidalira mwaife tokha plz. President sangayendele galimoto ya 10million osatheka ndchfukwa ali presodent. Sionse omwe akuvutika ndi njala ayi kodi bwanji? Olo akanagula chimanga cha 100m yomwe mukunenayo akadyetsa miyoyo ingati? Olo baibulo linanena kale kuti aliyense azadya thukuta lake we hv to work hard rather than relaying on government for help. Work up my Malawi plz¡!!!!!!!!!!!!!

    1. Mr. Anthu m’dziko lino amazidalira okha ndipo anthu amagwira ntchito zotukula m’makomo mwawo mwamva, koma sizingaphule kanthu kapena kuti anthu sangatukuke ngati boma silipanga zitukuko zopindulira anthu ambiri

    2. Koma blaza izi ndzizindikilo zosonyeza kutha kwa Dziko tingovomeleza basi maiko onse zavuta tisalozane zala thanks for your point bra

  198. Do u pple remember wat ur mbz was saying wen de some pariament aprovd the buying of 3 vehcz for speaker leader of opp and depspeakr lets put politics aside and talk issues here buying him a car is nt wrong as long as we hv medicn n hospitalz unvecty are open pple hv food pple hv mony bt doing it now mmmm i dnt knw how can one be claping hand for dis

    1. If you don’t have food it’s your laziness, even Kamuzu MHSRIP was telling us to work hard in our fields. Don’t always rely on the government. Politics should be pended to 2019

    2. Mukamakwanitsa kukhala pa fb kumayakhula mokhuta muzidziwa kt ena akuvutika ine mutha kundinena idnt mind coz u dnt knw me koma alipo ovutika yemwe mukumudziwa anwe God z watching zonse tikupangazi

    3. Amene mukuwadziwawo athandizeni man osamangokhala ndi mtima wachifundo poyankhula koma kuchita kangachepe mumapezako gawirani anzanu choncho muzalandira madalitso ochuluka komanso osamayankhula zinthu chifukwa chandale

  199. Tangoganizani president wamzeru angapange zimenezi mmmm galu uyu wanditopesa tsopano look Tanzania is now a better country coz of president Mwangufulusangatengele chisanzo chimenechi apa mbuzi ndi zimene zinavotera

  200. Enanu mudazolowera kuyima pa msewu ndikulandira k50 mukukanika kugwira ntchito mukuti president azikupatsani, mwagwa nayo musiyeni anjoye nayeso ulesiwo ndi wanu anzanu akulima madimba ndikugula ma galimoto uko osangolongolola apa.

  201. Komanso apa inu palibe galimoto yoti mpaka kuyikambila nkhani tazaonani ma bwana amene ifeyo tikwagwilila ntchito pa jozi pano kuti akuyendela ma chine antundu wanji koma amalawi pali chinyani apa nanga akanagula ndege nde mukana fentatu bullshit

  202. So wht is the problem u guys? The car is for the president, and the president is working for pple. Are u sure that million can feed all malawian for their lives forever? Pls wak up and defend your life yourself. And u Malawi 24, is that all Malawi last news to post?

  203. So wht is the problem u guys? The car is for the president, and the president is working for pple. Are u sure that million can feed all malawian for their lives forever? Pls wak up and defend your life yourself. And u Malawi 24, is that all Malawi last news to post?

  204. So wht is the problem u guys? The car is for the president, and the president is working for pple. Are u sure that million can feed all malawian for their lives forever? Pls wak up and defend your life yourself. And u Malawi 24, is that all Malawi last news to post?

  205. Kodi mutundu weniweni wagalimotoli ndi uti?Ena mwaonetsa white ,ena awonetsa black ena meroon which z which?(colour) kkkkk

  206. Agule bas kapena inu mumafuna mukwere nawo? Lembani ina zopanda mutu izi mumafuna akugaileni ndalamazo? Kkkkkkkkk anabwera2 paja mumamwalilisa ali moyo pano mwati mukambe ina kkkkkk zamanyazi LONG LIVE APM if i wz the owner of fb page iyi ndikanalithesa

  207. ndiwodzikonda sasamala za amalawi mwina afuna ma demo moti ndalamazo sangapeleke ku escom kt iwathandize ndikundandizaso amalawi mwina kumati utsogoleri ukuwakanika?

  208. Ngakhale ine sanandilembe ntchito koma cndikudanfaula kut wagila galimoto nkachaniso kameneko mukanandiuza kut wagula Indian Ocean nkanat wandikanda pa dazi ngakhale ndilibe

  209. Ameneyu akufunika avekedwe tayala khosi awawapezelela amalawi he think there are dead people ndi munthu odzikonda bvuto amalawi

  210. ndinakakhala ine Muthalika ndinakagula even kuposa imeneyoa.I thought u pipo said he is died so what is it now?I don’t like politicians but the manner in which pipo treat this guy is not fair at all.Ndikhala ine njala nde even nthawi ya Bakili ndinavutika I can’t blame anyone.Its high time pipo must work and support themselves and stop blaming someone for their problemsa

    1. u can malawian help themselves when dey are paying a high tax km work yake osaoneka mdima tikugonamu wina ku magura galimoto its our money think very well

    2. S Gerald Sato, poyamba tipepese chifukwa cha English yanu. Kodi mungatiuze kuti msonkho mumapereka wochuluka bwanji.pachaka. Komanso vuto lakuzimazima kwa magetsi so president koma nyengo mmene ikuyendera zaka zimenezi. Nkana inuyo mutakhala president simungathane ndi mavuto one a anthu. Siyani ndale tiyang’ane chitsogolo, muchedwa nazo izi.

    3. Wachita bho ndipo wachepetsa anakangogula ndege. Metsa amati uzadya thukuta lako komatso iyeyo ali patchito. Mukuziwa kale inu athakati inu. Pompano inu nomwe mumati wamwalira ndie lero mwayamba yagalimoto. Kodi chimakhala chani kwenikweni abilimangwe inu? Abakha inu mmmm musandilaxwitsepo apa.

    4. basi chizungu chizungu, ndekt chani??? za chamba basi, inuyo mukumnena mzanu chonsecho nanu mwagundika kukomenta mu chichewa, zikanakhala kt sizikumveka nde bwez mukukomenta, tyeni uko agologolo achabe chabe inu, za APM muyankhula mpaka mutopa nokha, sibola iye wakwanilitsa zmene amafuna ku mtima kwake, muona ngat magalimotowo akabweza chifukwa choti mukumutukwana!! iyaaaaa!! lazy people!!! shame on you alllll!!!!!

    5. chifukwa ndi presdent ndye azifinyika? kapena dziko lonseri amadyesa ndi APM? njala yayamba chaka chino zaka zapitazo kunalibe njala? munthu uja akugwira ntchito yaikulu kutumikira inu nomwe ndye axifinyika ? mukakhala inu ndye kuzikundikira pamene neba wako akuvutika mwati tikudikira APM azathandize? ana anjoka inu even the bible saic”

    6. Civil Servants munapusa kulola 15%. Mwaona mukugwira ntchitu ndinu,iye angoyendayenda,mukapita ku chipatala kulibe mankhwala,iye ali ndi medical scheme kwawo kwa merica.

    7. Civil Servants munapusa kulola 15%. Mwaona mukugwira ntchitu ndinu,iye angoyendayenda,mukapita ku chipatala kulibe mankhwala,iye ali ndi medical scheme kwawo kwa merica.

    8. Kodi president mwezi ukatha samalandira ndalama?? mmafuna agule njinga yopalasa muzimusekaaaa??? njala yayamba lero??? mukuleka kulimbikira pakhomo panu kudikira president???

    9. Eti Gerald the little tikupeza akumatibelaso kuzera mumisonkho nde u say we shd start kumazidalira patokha? Ok. Asiyetu kudula misonkho tione ngati atagule magalimotowo?

    10. Akulanda kwa anthu osaukafe coz soap, muchere , paraffin ndi zina ndizina si momwe zikudulira pomwe if u compare with other countries nde zinthu cheaper kwambiri.

    11. Anga mvuto,iweyo ukakhala nazo ntchito mkupana mankhule amako akugona limodzi ndinkhumba kusowa pepala nyumba kudontha,ngati sugwira ntchito ikuphadi njalayo.

    12. Iweyo usamadule msonkho usiye ife tizidula umafuna president azifanana ndi ambuyako kusauka?Nsanje basi mapazi obookawo kalijosolo wachabechabe

  211. Sindine wandale koma palibe cholakwika.pali olemela ambiri akusintha magalimoto chikhalilecho azibale awo akuzunzika.NDE yilakwe ya mtharika be fair guys.

  212. Next time uzigulire jet mr president! Zagalimotozo ayi. You are the President though you are leading weak people with fable mind. Za President eti zikhale zao nde galimotoyo inakadyesa mtundu wa a Malawi, kuyakisa magesi 24hrs kubwelesa madzi ndi zina ukuganizazo admin? Kufuntha, vimbuza!

  213. Palibe nkhani apa amalawi tinakhala bwanji? Munthu agule ndege ayi agule galimoto ayi koma agule njinga yakapalasa ndiye mukondwa, Munangokula ndi moyo wansanje basi

  214. Admin plz try to publish stories which will benefits viewers of ur so called News24. Two much unnecesarry stories

  215. parliament agreed tu buy tht car…..zimafuna kut amalawi muzitibalalitsa ndi tikhan tanu topusazo tithe….pena mumalemba zanzeru…koma pena u only tryn tu confuse poor malawian….its tym we sae no to stupid publish…nonsense

    1. That’s my point: where were these people (including Malawi24) pamene parliament inkapanga approve the budget for the purchase of 8 vehicles? Kungofuna kusokoneza a Malawi basi

    2. Amwene 100% Chifukwa Amalawi 24 Angolemba Zotha Itha Komwe Amagwilizana Kunalibe So Ngat Adagwilizana Nazo Kut Azamugululira Magalimoto Sizitengelanso Kut Kod Tikudutsa Mu Nyengo Yotan? Agule Bas

  216. jah know mi nuh vote again, y Present turn their own country ppo into refegee??? Malawi still poor ppo land, y buy expensive car while ppo whom voted him to b a leader suffering in food, kaya ndalama ndi zake komabe amayenera kuganizira anthu ake! Kusatiganiziratu kumeneku!!

    1. Palibe galimoto apa mpaka kuyikambila nkhani anthu ntauni muno ya jozi komanso anthu akenso akuda akumalawi konko akuyendela de some machine why we making blah blah for nthing

    2. galimoto yake iti? this car is cheap and the rest 7 cars are not bought but you are still complaining? wake up Malawi and work hard so that u can stop talking nonsense

    3. feed family then dress up yo self guys! jonz yake it?? ifeso tiliku kuli ma galimoto koma u can buy expensive car while ppo who voted r suffer

  217. Musalile ino ndi nthawi yake yathuyo ikazakwana azativa, koma musasiye kumulangiza azinyozela yekha, paja amati timamunyoza.

  218. Vuto nchani??? Samalipilidwa? Lets learn to publish stories which will help curb our problems otherwise puting blames on others doesnt change anything

  219. Guys tidzikhala anthu achilungamo nthawi zina.Parliament inavomeleza bill yogula galimoto zatsopano za president .sananene mtundu wagalimoto yake,now galimoto yagulidwa tayamba kulongolola why why?this was already budgeted .kodi ndalama imene yagula galimotoyi ikanagula chimanga chodyetsa amalawi tonse??.Lets be reasonable sometimes.Mbiteee

    1. Umunthu Ndiofunika Kwambiri Olo M’mene Parliament Inavomeledza Kma Umunthu Alibe Cfukwa Akanapanga Divert Ndalamazo Ndikupanga Zinthu Zotandidza Mutundu Wonse Wa Amalawi.Iweyo Ndamene Udzipanga Reasoning,ukundiudza Kti Nyumba Yako Ana Akufuna Nsima Basi Iweyo Ndikumagula Plazma Eiish Tidzamaone Zonse Akupanga President Z Rit No

    2. #Roosevelt dzina lako landikumbusa history poti waku USA anali wanzeru moti fundo ten zomwe anapeleka kudziko zinathandiza…iweso reply yako ndiyanzeru…..bambo osiya kusamala banja lake kupanga zozisangalasa yekha ndekuti ndichisilu.reasoning akunikadi iwowo.

    3. Koma anthu akudziwa zimezi akulu? Ndinu nokha amfumutu mukudziwa zimenezi. Ndi chifukwa chake Malawi ili pa mavuto. Wina akagula wochi yabwino, ooohhhh.. ndalama zathu zija amwene. Tatiwonetsani za gulu… kkkkkk

    1. Uyambe wadziotcha wekha, udziotcha bwino galimotoyo, wagula ndi ndalama yako? Kod kumudzi mkut? Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk amalawi osayamika inu

  220. If you want him to use the car that anyone can use. Then we don’t need to have a president . Please leave the president to be a president don’t compare president with mr whatever you call them Achisale , aphiri, ambewe or ajere. So don’t be jealous.

  221. Mind u ESCOM, Water boards, ADMARC and all MDAs have their budget lines and they spend according to the budget plans so is the State. So if some services are not efficiently offered the blame can’t go to anybody else but the CEOs of those MDAs. Mind u parliament approved the purchase of 8 presidential convoy fleet if anything we shud blame our greedy parliamentarians for not shooting down the budget but just passing it. Every budget needs to be implemented and I just thank APM becoz he has just approved the purchase of just one vehicle leaving the other 7 I hope there is sense from his nonsense

    1. So that’s the problem with u coz suli kwathu kuno so leave us alone though kwanu sikudziwika otherwise u will just bring shame to ur arguments

    2. Dere is no car dat we cn make blah blah here it is de cheapest car to compare D A president is using not zuma why we r blaming for nthing dis car is de same lyk de one he is using sundows player #Teko Modise

    3. only lazy pipo lyk ndiomwe akulimbana ndi mr p, winawe chipulumuso chikazakupitilira uzati yesu ndiokondera. Konza mtima onyansawo uyang’ane kumwamba ndikomwe kuli mayankho ako onse

    4. No don’t give such an assignment, just google urself and bring out the meaning and the relevance of that meaning to this issue at hand Mr Givah

  222. bas kagalimoto kamodz kokha? nanga akadagula jet zikadatha bwanj? akunena kt akadathandiza pavuto lamagetsiyo akunama. tazolowera ife kukhala mudima, sizachilendoso kwa ife zimenezo

  223. Inu mukukhala ngat amuthalika simukuwaziwa bwanji?bola pitala koma bingu suja adagura zima hummer munthawi yonga ngat zomweyi?

    1. bodza man that time Malawi economy was on number one fastest growing in Africa. Where were you? I remember that time I was enjoying life so much. but those stupid and greedy opposition politicians pull him down

  224. Za zea! Inu mutakhala Prezident muziyenda wapansi???? Inu njalayo waibweresa ndi iyeyo?? Kuvuta kwaMvula amapangisa ndi iyeyo?? Galimoto ndi njala pali mgwirizano otani??? Padakali pano ku Thyolo kuno anthu asiya kukwera njinga za kapalasa pafupi fupi khomo lina lililonse anthu akupezeka kuti akugula njinga za Lifo zawandazi achina Bwamnoni mkati njalayo ili choncho! Ndiye mukutanthauza kuti prezident akhale opanda galimoto??? Za mkutu eti paja ndi inu nomwe mukafalisa kuti wafa!! Bwanji osamafalisa zinthu zoti tizipita pasogolo??? A Malawi nsanje tifika nayo pati???

  225. A malawi sanje chabe munthu amusiye mwina ndi ndalama nzake munthu mmmm let him enjoy dis lyf kukhala president sikuti atidyesa tose ayi kma manongongono basi kkkkkkkk

  226. EEEEEEEEE Paja Kubadwla Kumalawi Ndkulimba Mtima Moti Peter Asagule Galimoto Coz Ndpresedent . Kod Amalawi Munakhala Bwanj Uchitsilu Okhaokha Basi .Ndakwya Nanu

  227. Koma aMalawi 24 muli ndi vuto. Hahahaha. Pali nkhani apa? Mumafuna 1st citizen aziendera galimoto ya 19gobede yomweyo? Ng’o! Mukhaula

  228. Kod ndalama imeneyo mundiuza kut ndiyomwe ingathese mavuto ali kumalawiko or magetsi kkkkkkkkkk zopisa basi kumazolowerako moyo wa ovutika omazidalira pawekha osati udikire peter azakupatse chochita , mbuzi inu a anyasa 25 ndi omwe amakutumaniwo

  229. big up mr president, life too slim..,.. Ndi dollar zake munthu musiyeni anjoyele nsanje bwanj., muona ngat umphawi ngwa tonse?

    1. Eti eti amada galimoto zoti ukakwera kumaona nthaka.president azidemelera ka.ikakhala njala yagwayi ndi nthawi basi,asanamizire president

    2. Akuenela kugula, ndim’bale wanu? Kukhala president sichifukwa, mudzilima chimanga chambiri musamabvutike ndi njala musiyen adziusumana aa-aaa

    3. Walakwisa kugula iyaaaa palibe zonyengelera kuvuta kwa magetsi’ku sakukuwaona enafe timadyera mu business za magetsi, panopa 1week yatha kulibe magetsi kwathu kuno ndiye mukuganiza kuti tizidya chani? Ndiye anthu mumvekere eeh mukufuna boma lizikudyesani pakhomo panu, ndiye kulankhula kwa mtundu wanji kumeneko? Anthu’tu amagwira ntchito zozitukula okha ku Malawi kuno koma samapeza phindu chifukwa chazochitika m’bomamu

    1. Akanagula jet koma kugula zotchipa ngat zimenezi amalawi mumadziwa kutsusa koma kuyamikira pakachitika chabwino kumavuta

Comments are closed.