A Malawi akwiya ndikuletsedwa kwa chakumwa cha Frozy

Advertisement
frozy

A Malawi ambiri ati ndiokwiya ndikulesedwa kwa chakumwa chozizilitsa kukhosi cha mdziko la Mozambiki cha Frozy.

Kukwiyaku kukutsatira zomwe lanena bungwe lo unika zinthu mdziko muno la Malawi Bureau of Standard (MBS) dzulo pa 25 Okutobala kuti chakumwachi ndicholetsedwa mdiko muno.

Bungwe la MBS lati mumchakumwamu muli tizinthu tina tomwe sitikuenera kukhala muzakumwa ndipo izi zapangisa bungweri kuti liletse chakumwachi.

frozy
Chakumwa cha Frozy chaletsedwa.

Mwazina bungweri lati lizipereka chilango kwaonse opezeka akumwa komaso kugulitsa chakumwachi, ndipo izi zakwiyitsa anthu ambiri mdziko muno.

Poyankhapo pankhaniyi yomwe inaikidwa patsamba la nyuzipepala ino dzulo, anthu ambiri ati izi ndizoduka mutu.

Iwo atiakuganiza kuti bungweri latumidwa ndi kampani yopanga zakumwa ya Carlsberg kuti alaletsa chakumwachi kamba koti kubwera kwa chakumwachi kwapangitsa kuti malonda azakumwa monga fanta komaso kokakola avute.

Mmodzi mwaotsatila nyuzipepala ino a Steve Mumbulu anati “MUKULESA FROZY PAMENE FANTA WAKUMALAWI NDIWOKWELA MTENGO NGATI MADZI OPANGILA MUMACHITA KUWODETSA KUNJA.MADZI OKHA MPAKA K250 PAMENE FRONZY K2OO NDI BOTTLE LOMWE. ZOKUMWA ZAKUMALAWI NDI ZODULA KOMANSO ZOSAKOMA.TAX YACHANI PAMENE NDALAMA ZA TAX ZINGOBEDWA IFE TIZILIPILA NSOKHO INU MUZIBA FROZY NDI DHIL NDIPO MUPANGE MA 1LITRE TIZIMWA BASI NDALAMA NDI ZANTHU..”

Anthu ena adzudzula bungweri kuti bwanji likulora mowa ochokera ku Mozambiki konko kumagulitsidwa kuno kwathu ku Malawi ndipo ena anaonjezera kunena kuti frozy asaletsedwe chifukwa sanachotsepo moyo wamunthu komaso palibe banja lomwe wathetsa.

“Ndimabanja angati omwe frozy wathetsa, ndimoyo ingati yomwe wachotsa? Bwanji nanga sikuletsa zakumwa zoledzeletsa monga mkalabongo, sibwino. ” anatero a Mary Chatha.

A Frank R Meleka anati ilindiganizo labwino ndipo anaonjezera kuti “KOMA ANTHU ENA NDINUDI AMALAWI KOMA? INU MUKUKHALA NGATI ANTHU OSAPHUNZIRA BWANJI ,JUST GO TO TZ ZAMBIA IF YOU CAN GAT A PRODUCT YA SUN CRAEST ,KUNGOPEZEKA AMAKUFUSA MAFUSO OVUTA KUYANKHA WACHOKA NAZO KT ZIMENEZI KUNO AYI,KOMA IFE KUNO TIMANGOLANDIRA ZILIZONSE.

Mwa anthu 500 oyambilira omwe anaikilapo ndemanga pankhaniyi, anthu 487 anati ndiokwiya ndi kuletsedwaku pamene anthu 7 anayankhula zosagwilizana ndinkhaniyi ndipo folo otsalawo ati kuletsedwaku ndikwabwino kwambiri.

Advertisement

341 Comments

  1. Achita bwino ukamwa imakhala ngati wakhuta pomwe ayi acid yekha yekha atiwononga. Ambiri akupezeka ndimavuto ochuluka kwa acid kamba ka frozy. Fanta ayambe kuyika mabotolo aprastic yobweza botolo uli pachangu ndiyowawa. NDE khani

  2. Coca-Cola being the best in quality and employment accept the good idea, you killed BAt, pew, enco, Bandc but you never learn

  3. Why Do Government Take Time To Ban Things Which Are Bad To Malawians? That Drink Is Not Good At All That Is Why It Is Cheap. Think Twice When Going Things

  4. Amalawi ambiri kusazindikira, akuletsa kuti izinzoipa inu mwati iyayi zoipa zomwezo ndiye chani amalawi mtundu wanga

  5. Nsanje boma ili bwanji? Fanta wanuyo ukagula ndi gaba npaka mabotolo atatu gaba osatha pomwe flozy nmodza agaba awili amatha komanso ndalama yochepa. Botolo lakonso kupita nalo kunyumba. Amalawi tichitepo kanthu apa atipweteka ndikutenthaku wayambitsayo ndi nfiti yamunthu mulungu amulanga ndi2 ndalumbira ine sindimalumbira wamba ziwoneka mumudziwa. Flozy wooooooooyeeeeeeeeeeeeee. Fanta kudula kuti ziiiiiiiiiiiiiiii sheeeeem!

  6. This is painful to poor Malawians! Let’s support each other by getting a court injunction and our court make a ruling on the matter.

  7. malawian products too much expensive & poor qaulity thats why most malawians are after foreign products that are high qaulity and affordable price ooh!! sleeping regime that i never been seen before there is competetion on world markert malawi wake up please

  8. Osaletsa kugulitsa shooter bwanji yemwe akuononga nkhope za achinyamata ambiri,anthu angonenepa nkhope yokha kuli kutupa ndiye mukaletse zokumwa zomwe anthu ambiri akuzikonda kamba kaku cheaper Malawi wanga sadzatheka ndithu

  9. bwanji osaletsa mowa coz mumapezeka acolholic substances, SOBO company yachita katangale ku boma, tizikamwera ku mocambique konko. Foolish

  10. You cheap MBS you v failed to ban nkhoma water project which supply unsafe water to the community containing feacal matters.You must be serious start with your home product s . Frozy watani bodza lanulo where were you at de very begging. shame on you. If you are serious come to nkhoma and ve some tests on this water project run by un qualified south african national.

  11. Apa zikutsonyezeratu kuti aSobo mukulephera zinthu zanu? Ma comments ali apa akukamba za frozy kuti ndi wabwino…. Olo ko vota timayendera majority…… Apa frozy wawina abwerere. Chili chonse chopangidwa ku malawi ndi chodula, ndichifukwa timakonda zakunja

  12. Ndipanga mademo anga ndizavula nkuvala panti yekha wa green ndipo ndipempha ma concerned frozy people to join with your pant of ur favourite frozy tikafika ku mbs. akulesa frozy pamene zakumwa zomwe anthu akufa nazo ayi. shooter black ponder munaikisa mmabotolo koma anthu akufa nazo. muhahahahahahahahahahahahahaha

  13. Chakumwa chabwino gat chimenechi chalakwaj?chonsecho ana anu ku school akumwa frozy wa green,mwatitola ife tidzimwabe zanu zimenezo tisiya pokhapokha mutiuze chifukwa chenicheni.

  14. Ma mozambiki ndi maneba, ndie ayambe kuwauza kt aneba zimene mumapanga mutha kuononga nazo anthu, osati kuuza anthu ogula ndi kugulisa, yimeneyo ndiyo tmat nsanje.

  15. Nyasaland,,,zonse zachikalekale,khalidwe,umphawi,umbuli zosasintha,dziko kumangolowebe pansi chilichonse chovuta,,frozy walakwanji?

  16. Kodi bwanji Coca-Cola Mozambique sikudandaula.akuchulutsa kudandaula ndi coca cola malawi zikukhala bwanji jealous siyabwino amalawi ndichifukwa tili anthu ovutika

  17. Kuteluku muli unama zedi uyo amene onena filozi aletsedwe sanali ufusa ife weni nthaka, kuti ove nkhawa zathu, theladi onene dzifukwa dZokwnila utelo, ndili unena yapa fata situli ukwanitsa kugula,olo ingoitanani kampani yophika filozi ibwere idzapikisane nawa anzathuwa mwina dele nawoso oyesele usitha mitengo,ngatidi muliunena zoona uzeni zifukwa zookwanila

  18. zabwino sizichedwa kuthadi eti ,osaletse timowa tamasachetiti bwanji. Achina black punch,shooter,, sobo botolo lanu lija ukamwera lero wina akamwereko kunathenje tsiku linalo kwa biwi, frozy ukumwa botolo umataya…

  19. Inenso Ndili Okhumudwa Why Gvt Osalesa Win,joy,charger Ndi Azizake Amene Akubwele Mavuto Oonekelatu. Ah Ukusikuletsa Koma Kuitanila Malonda, Ine Ndizimwabe Frozy Tipeza Njira Tizigula Ngati Mmene Amaguli Chamba

  20. kma mw 24 ngati muķutumidwa pepani musatisongoneze ife anthu akumuzi anakalesa ntobwa kpena kti thobwa tinakadandawula zimeneźo ulo áyini moshiko samwa kudederuka bansi nenaniño zá mipingo nsano plz lathu ndilámkáka ndi uchi musatisoñgoneźe plź

  21. Malawi will always find a way of blocking something that is more helpful and affordable to the poor people. In early 2000 there used to be some soaps (Orchard as it was written) from Zimbabwe and sugar as well. These things were much cheaper than our local stuff regardless of their custom on the way they met. But the government quickly came up with their own explanations to bar the poor nation of buying the stuff. If there is no competition for customers, how can we expect price drop?
    We know the government wants to help home industry but the best way to do that is by considering the lives of the people it serves.

  22. ZIKUONETSA KUT TIL MMASIKU OTSIRIZA.BOMA PAMODZI ND A MBS AKULIMBANA ND AKHILISITU POWACHOTSERA CHAKUMWA CHIMENE AMACHIKONDA. KOD AKUFUNA KUT NAONSO AYAMBE WINE ND ABALE AKE? ZOMWE ZIL ZOOPSA PA MOYO WA MUNTHU? THINK AGAIN MALAWI WITH UR FOOLISH MBS.

  23. vuto la amalawife sanje eyaka

    inu kufuna kudula chonse umphawiuliphwiiii

    ndani atagule zodulazo tilidola

    stupit

    frozy alibe zomwemukunamazo

    jst say

    ndiwotchipa and it affordable
    by the great dmand than zanuzo

    sanjerekaa mbufwiiiitii mulinawoooo

  24. If it iz like tht then mulesenso ufa wa Zambia umene anthu ukutipulumusa pano n Oranges zopanda nthangala zija n apples,, mukumangopanga ziganizo osawafunsa anthu bwanji maganizo awo????

  25. I would love mg to talk to the company in Mozambique to have an authorised outlet depot in Malawi to distribute this drink and reap the revenue wanted from it…osati kuletsa sheeeeeeeee

  26. Chofunika apa company ijayo ikugulugushayi ingoika pa low price kuti ziende bwino

  27. What about Chinese products which their description is Chinese? ,which majority of us we cannot read even a single word …. shame on u!!!!!!!

  28. Amalawi sitingatukuke cz of jelous bwanji anthu akukwiya ndkuletsedwa cha frozzy yet is not energy drink pamene tili ndi product athu eg fanta coca-cola let buy and improve ur beautiful country.tikamagula maproduct anthu means ambale athu alembedwa komanso tikutukula malawi wathu.

  29. a malawi dzaçhibwana batsi ndi chifukwa zikomuno uphawi suwuzatha jelasi ķwambili zokumwa zàbwino mumàdaña naźo komaso zoshipa ñģàkhale mwalesà zanuzo siđzingayeñde malonda mumaduĺisa kwàmbili zoti zikolathuli ndilosauka simuwa àyi mwachita bwiñotu mwalipatsa mwayi thobwa tizimwa thobwa palibe angamwe zoduĺa źoshipà zilipo mwàyi wathobwa sopano ķkķkkķkķkkkķkkkkkkkk

  30. i am surprised why mukudandaula anthu inu… kodi zakumwazi zimwabwera munjira zoyenera? otherwise chuma chonse cha ku malawi chikumapita ku mocambique

  31. Ilove Frozy Zanuzo Ukooo Zakumwa Zozizilitsa Ku Khosi Zmachta Kusowa Mukufuna Mukawathamangtsa Tizifa Ndluzu Sichoncho?Zanu Mukapanga Nde Mukagulitse Kunja Inu Mwatan Inuyo Kutchuka?Ziko Lauve Losowa Maz Nd Magesi.Musanaletse Mundfunse Kae Ine Ogula MBS Mwahongedwa Nd Asobo?

  32. When Jeolousy Grows, Cruelty Followsuit And Reigns.Mwina Aku MBS nanunso mwamwako mwaona kut vuto lenileni ndi chan? tidandaule nd MBC kenakanso MBS?

  33. MSB Should Be Serious.Do Standards Also Apply In Malawi.Talk About Something Else.Ife We Are Used.Its Not Only,timangozidyeradyeratu.

  34. Abwinodi sakhalitsa zoona iwe frozy wapita kusiya win,shooter,kachasu,mkalabongo zomwe zinabadwa iwe usanabadwe sob sob ai mzimu wako ukause

  35. Ine kumalawi kuno kumandidabwitsa kodi zakumwa zimenezi zabwera liti? Mudatani kuletsa atangofika kumene ife mkamwa mudazolowera kale sitileka, fanta sitingakwanitse ofunika nduna, zimakhala zodabwitsa kuti zithu zakwathu konkuno koma mtengo okhawo eeee kumati akugulitsa kapena akukaniza nde muuzane amene munabwera mfundo yoletsayo kut na ine ndikadamwa kaya muletsa ndizikamwera ku mozambique konko

  36. What standards are they talking about? People collect the empty bottles of frozzy and put water,thobwa and sell what standards are there? What standards are there in soya pieces where my friend found a dry lizard?What standards are there in dzitumbuwa, freeiizes we make in homes?But Malawians still survives. What standards are there in our stinking taverns,resthousez, do we really have Malawian standards? Frozzy has killed southern bottlers be realistic…running away from competition

  37. I think its about time the government realises that Malawi is not a dumping site for counterfeit commodities!
    A move in the right direction, hands up!

  38. Problem with Malawian ppo,,w av alot of lands wher mitsinje ilipafup n akhoza kumachta irrigation,,atazala fruit trees in which,,they can av zpangizo zopangra juice or any other fruit juices,,or they can sell at those companies amapanga ma juice wo.and nkumagullisa kwaamalawife at a fair price evn exporting the products.alipo apa anthu aagriculture,ma advicers,,smungapteko kumalo omwe kuli mitsnje but ppo r not using it?iwent kuthyolo the other tym,,i could c ppo sweating kuthirira mbeu yet the rivers r too far from their gardens and paja its a high area,imagn.

    1. Kumasenza madz from the nearby rivers or dams kumathirira,,n if alibe machines opangra juice yo ndanena kale kut kumalaw kuno aliko ma company omwe amapanga zmenezo,,iwo akhoza kumalima n nkukagulisa zokololazo.n panopa kuli shoprite nd ma shop ena nd ena omwe znthu ngat zmenezo zmagulidwa bwno,,ma fruits n juices.as fo me,av worked in a nursery before,n i realised that kulima ngat znthu zmenezo nd deal.so yes awl invest in farming,ofcoz am also a student in education,but not in agriculture.awl mek sure i reach those areas n advice how important t z to do that.i c ts not only agriculturalists who can do that,evn ppo in other fields can,wt help ofcoz from agriculturalists.evn in those lands wher gvment owns,,they too can do sometn about t.awsh they c how other countries do t,,using tha type of irrigation…

  39. Ine ndidamwapo komaso sindidamalizitse mmh sizilibho zilibho kuletsa asaaaaaaaaaa. But i understand that pple cannot accept the ban bcoz frozy ndiotchipa & they don’t care kut muli acid wambiri.

    1. Mmmm inu??? Y nt kupanga barn cigarets that gives complications to de lungs end it z more dangerous than ordinary frozy. Osamangowombera m’manja zilizonse. MBS mmmm?? adyapo

  40. Aaaaaa koma malawi abale malawi sazatheka basi aaaa kaya zikwiyani ndi frozy yo kumalawiko ndizanu zimenezo ine bas kuno ku jonzi zangaphe ndi zakumwa zonchipa achina cokacoka 2litre achina fanta 2l,lemon twist,granadila twist,spaleta,kingsley,refresh,mirinda,twiza,coo-ee,pepsi,7up,appletiser and sprit.zakumwa zonchipa ma ma 10 rand,15 rand kumwa ndikuzilephela kamba kochuluka osati zakumalawinsm somdula komanso zochepa

  41. Mbs is not realistic on the reasons for barning frozy. If mbs if worried about peoples health upon consuming frozy it would first barn the selling of cigarates which are naturally health harzurd. Tobacco is known of causing lung complications, barn it first. What is realy the motive behind the barning of peoples choice frozy?

  42. First stop Coke because is a toxic drink. It is acidic pH2. Almost similar to hydrochrolic acid in a battery which is pH1. Thats nothing but Jelousy of foreign drinks. Malawi got alot of fruits but failing to produce cheaper and heithier juice. Stupid Presidents and ministers. Stupid leadership. What you know is cashgate and hiding a sick president.

    1. Kikkkkkk sounds funny but there’s a sense there, aletse coke, coke galimoto kubode ngati kunali dzi oil kungotsukila coke dzimachoka, ndiye mmimbamo amapanga zotani? useless ppo, aletse kaye coke ngati akufuna

    2. Inu mukunena coke….xotsukira toilet…kuteroko ndufuna ndikayese frozy ngat angachite xomwe amapanga coke ukatsukira toilet….at high acidity ngat zinaz zilibe acid…kkkkkk

  43. MBS!!!!! U HAV BEEN BRIBED ???!FOOLZ.SOBO HAV U BRIBD???.FOOLZ.GOVT HAV U BIN BRIBED????FUL OOO SHIT IWANTED TO SAY FROZY U WIL BE FROZED.WAIT A BIT.THAT {FOOLISH AFRICAN NEVER TAKE ALCOHOLS,FANTA}WIL FROZY TOO!!!!!!MULETSA FROZY TMAGULA NDIFE FANTAYO MUGULA NOKHA?????ZINA KUMAGANIZA KAYE MUSANAPANGE OSANGOKHALA NGAT MBUZ ZA STD 1.BWANJ TKAKUMANE KU MOZ KONKO TKAMAKAODA?CIVIL WAR YA MALAWI IKAYAMBIRE KONKO.

  44. Kodi ku Mocambique ndi ku Malawi kuno kuli athu osiyana matupi ? Bwanji aku Moshco sakudwala or kuletse kuti asapange? Even Coke ali ndi Gas wambiri

  45. Kodi Ana Akakondana Makolo Amati Chani?Sibasi Alekeni?Ndie Amalawi Ndi Frozy Ndi Khethe Khethe,tsono Inu MBS Mutichani?Ingokambilanani Ndi Company Ya Frozyo Kuti Angochotsamo Zosafunikirazo Basi.Ife Ndie Tilipa Mbuyo Pa Frozy.

  46. Drink la acid ngati ili sinalioneko mmmmmh ,alichita bwino kulibana,,aaaaagh chirichonse cha pa botolo mu chiphwitikizi zachamba,,aximwa aphwitikizi omwewo,,nde wina uzindinena kuti anakutuma ndani kuti umwe ,,nde kusaziwa zabwinoko kumeneko,,,

  47. Kachaso wakukanikani kulesa chonse akutenga miyoyo ya anthu nde mkulesa chakumwa chabwino bwanji?asiyeni anthu amwe zomwe zikuwakomela

  48. Akutaya nthawi ndimaganizo opusa.vuto la kumalawi kuno sadziwa kupanga zakumwa zabwino komaso zotchipa.anthu amagulitsa chamba fodya oretsedwa what about best drink like frozy? timwe basi

  49. Wel done malawi poletsa frozy!.Muwauzenso amene amapanga cakumwaco kut abwere ku malawiko azikapangila komko apo ayi,akagwere komweko mzque.Malawi ngati dziko musamalore zilizonse kuyala maziko mdziko lanu pamene zachimalawi zikukanidwa ndi maiko ena.COTSANI NDALE KONDANI MOYO WANU NDI ZIKO LANU!

  50. TS AL BUL*****T TO MBS N GVT.KUT FROZY AYAMBE KULOWA MUNO ANAGOGODA KHOMA LA MBS NAMUVOMEREZA LERO AKUT SIWABWINO.ARE SERIOUS?JELOUS BAS MBUS.TS LYK WAT U DID WTH SUPA MAHEU FRM ZAMBIA.U HIKED T TIL WE NO AFORD T TODAY.NOW U HAV TURNED FROZY.I WAS DRNKN ND SELING T.TODAY 3300 COM TOMOROW 4000 CHOLINGA TGWE TZTUWA KWANU SMUTPASASO GANYU.F****.

  51. Fanta 300mls-frozy350mils…..fanta k250-frozyk200…..fanta the bottle is returned after using it-frozy we carry the bottle home….so is it balancing ???nyengonso yotentha ngat zino simomwe fanta,,coke etc zinkasowera….zachamba bax

  52. Kawilikawi inu amabuzneez mukumanyanya mukulemphela kutukula kwanuko koma kulimbana ndizinthu zakunja achita bwino

  53. frozy is good it does nt require alot of money in short it is cheap….u will never be asked a deposit wen buyin it,we malawian we lyk it…it quantity is more dan fanta n therez difference ov 50ml shopkeeper bring frozy oh sorry mbs hz barned it

  54. Tsakuwaona maiko enawa akupanga zozizirisa kukhosi malinga ndi nthumba mwa munthu kuli original komanso fongkong kuti aliyense akwanise kugula. monse mudayambira fanta ndi koko. ndi kale sinthani please

  55. TAKWIYADI,CHISAZO,FANTA,KAPENA COCOCK,350, UKHALESO,NDI BOTTLE LAKO,POMWEZITHUZO,ZIKUKOZEDWAKOMKUNO,KU MALAWI,POMWE ZA MOZAMBIKIZO,NDI, 250 230,TIZIGULAZAKUJAKO,

  56. Iweyo ndi amene wakwiya munthu aumunthu akwiya bwanji ndi kuletsedwa kwa frozy ngati ndi chakumwa chopatsa thanzi komanso chabwera liti ine mchewa weweni namti inu ofroze kwawo gule kwawo gule mangani vikwatu vanu ulendo uko kwanu ku Kilimani Ku Mazambiki

  57. Kakaka mitengo yodura thats y anthu akuthamangila zotchipa maluzi pamalawi akula nde option ndi frozzy malingana ndi kupeza kwathu botolonso sitibweza komanso amakhalamo ochuluka palitu zakumwa zambiri zokhala ndi citric acid wambiri malambe juice ;bwemba juice;kumbucha ndi zina bwanji sizikuletsedwa?this is october zakumwa ku SOBO mbuyomu sizimafika mwenzi uno zimakhala zatha koma pano zili phwiii meaning anthu akukonda frozzy zomwe zapangisa MBS kulandira dipo frm SOBO kuti apezere zifukwa zomveka bwino frozzy ndicholinga aletsedwe nanga kwao ku mozambique ko mmene ankazipanga approve sadawone mabvuto mudapezawa?nanga kuchipatala mwalandira odwala angati omwe adwala atamwa frozzy?

    1. Kkkkkk zopha anthu sakuzidziwa mafuta oyeza akumayamba kuwilitsa mmakonde mwa ma shop monsemu akumaziumila mubotolo mommo asanafike panyumba akutidwalisa ma hbp ndi zinawa bwanji sakuwalesa ku lidzulu ndi ku nayuchi komanso muloza border daily pansi pa minibus mmipando asomekamo zigubu zikulowa mma town mu apolice angolandilapo tima pin tonyenyeka bwanji dzaka zikutha sakuletsa koma akutipweteka mmatupimu

  58. The duty of Malawi Govt thru MBS is to see that people are consuming right things. If you feel that you can take what the Govt has abolished, plse do so at your own risk.

    1. goverment goverment! Which gvment.that one with cashgate scandles.work up malawi.boma lanu silikupanga zinthu dzothandiza ntundu wanu.koma mukukannidza okuthandizani malingana ndikusauka kwa dziko lanu.iwowo ammipando akumwa dzakumwa dzodula inu mzimwa ma juice opichila mmapepala.work up.be the nyasaland that we know.change that name of malawi because it is a cashgate name.remember

  59. Kodi ndi angati afa chifukwa chakumwa frozyy nanga ndi angati amene afa chifukwa chakumwa mowa wachilendo omwe ukukonzedwa ngakhale m’makwalalamu

  60. A Malawi ambiri ati ndiokwiya ndikulesedwa kwa chakumwa chozizilitsa kukhosi cha mdziko la Mozambiki cha Frozy.Kukwiyaku kukutsatira zomwe lanena bungwe lo unika zinthu mdziko muno la Malawi Bureau of Standard (MBS) dzulo pa 25 Okutobala kuti chakumwachi ndicholetsedwa mdiko muno.Bungwe la MBS lati mumchakumwamu muli tizinthu tina tomwe sitikuenera kukhala muzakumwa ndipo izi zapangisa bungweri kuti liletse chakumwachi.
    Mwazina bungweri lati lizipereka chilango kwaonse opezeka akumwa komaso kugulitsa chakumwachi, ndipo izi zakwiyitsa anthu ambiri mdziko muno.Poyankhapo pankhaniyi yomwe inaikidwa patsamba la nyuzipepala ino dzulo, anthu ambiri ati izi ndizoduka mutu.Iwo atiakuganiza kuti bungweri latumidwa ndi kampani yopanga zakumwa ya Carlsberg kuti alaletsa chakumwachi kamba koti kubwera kwa chakumwachi kwapangitsa kuti malonda azakumwa monga fanta komaso kokakola avute.Mmodzi mwaotsatila nyuzipepala ino a Steve Mumbulu anati “MUKULESA FROZY PAMENE FANTA WAKUMALAWI NDIWOKWELA MTENGO NGATI MADZI OPANGILA MUMACHITA KUWODETSA KUNJA.MADZI OKHA MPAKA K250 PAMENE FRONZY K2OO NDI BOTTLE LOMWE. ZOKUMWA ZAKUMALAWI NDI ZODULA KOMANSO ZOSAKOMA.TAX YACHANI PAMENE NDALAMA ZA TAX ZINGOBEDWA IFE TIZILIPILA NSOKHO INU MUZIBA FROZY NDI DHIL NDIPO MUPANGE MA 1LITRE TIZIMWA BASI NDALAMA NDI ZANTHU..”Anthu ena adzudzula bungweri kuti bwanji likulora mowa ochokera ku Mozambiki konko kumagulitsidwa kuno kwathu ku Malawi ndipo ena anaonjezera kunena kuti frozy asaletsedwe chifukwa sanachotsepo moyo wamunthu komaso palibe banja lomwe wathetsa.“Ndimabanja angati omwe frozy wathetsa, ndimoyo ingati yomwe wachotsa? Bwanji nanga sikuletsa zakumwa zoledzeletsa monga mkalabongo, sibwino. ” anatero a Mary Chatha.A Frank R Meleka anati ilindiganizo labwino ndipo anaonjezera kuti “KOMA ANTHU ENA NDINUDI AMALAWI KOMA? INU MUKUKHALA NGATI ANTHU OSAPHUNZIRA BWANJI ,JUST GO TO TZ ZAMBIA IF YOU CAN GAT A PRODUCT YA SUN CRAEST ,KUNGOPEZEKA AMAKUFUSA MAFUSO OVUTA KUYANKHA WACHOKA NAZO KT ZIMENEZI KUNO AYI,KOMA IFE KUNO TIMANGOLANDIRA ZILIZONSE.Mwa anthu 500 oyambilira omwe anaikilapo ndemanga pankhaniyi, anthu 487 anati ndiokwiya ndi kuletsedwaku pamene anthu 7 anayankhula zosagwilizana ndinkhaniyi ndipo folo otsalawo ati kuletsedwaku ndikwabwino kwambiri.

  61. Poorest country.. # 1
    Jealousy country.. # 1
    Cash gate country… # 1
    Electricity blackouts # 1
    & yet the warm heart of Africa (Malawi)

  62. Ineso ndili okwiya ndi zimene lapanga boma kutilanda frozy timalipira ana school lendi kuzera mu business ya furozy panopa mwaletsa muganiza. Kuti ife titani?

  63. just a good drink, osati simunabweretse ma empty. viva folozy. no need to return the bottle and defeating beautify malawi at the same time.

  64. pofunakuletsa (FROZY) kukhalakulakwitsa chifukwa ife ndife anthu osauka amalawi ambili ndiyechinali chakumwa chotsikamtengo komanso ngati ndimatenda ochokelakuchakumwachi tidatengakale komansondi osiyanamtengo cola .sobo.fanta.ndizodulaaaaaaaaaaaa.

  65. Litsen Malawians, we ve so many drinks the likes of yembe etc have not been banned. Has frozy been banned due to its affordability or it is not worthy for human consumption?

    1. If Its Not Worthy For Human Consuption, Then Our Govt. Is To Blame Becoz Frozy Analowa Kale Ndipo Ngati Ali Opeleka Matenda Ndiye Anthu Awatenga Matendawo.

    2. The fact about it is, these drinks find their way into the country illigaly, should the govt sit down and watch coz a lot of pple hv already taken it or come in the open to ban it n advise its citicens za kuipa kwake? Boma mpakana pano likukangalikabe kuphunzitsa anthu za kuopsa kwa HIV, tinene kuti popeza anthu anatenga kale nde ndibwino boma lingokhala osaphunzitsa anthu? Kupanda kuipanga ban drink ya frozy likamuimba muthu wina mlandu munthuyo akauwina mlanduwo kamba koti palibe fundo yolibakira boma kaa. Kkkk

  66. Letsani tilibe nazo ntchito chamba munaletsa silelo koma bwanji timagulabe mwaka n.bisalila momwemu ndiku makasuta ndiku tibandaso what about zakumwa zozizilitsa kukhosi nde mudzi enda khomo ndi khomo tu tikanamwa be dihlu ndiku iphenda chakumwa chosa bowola nthumba or muta nama kuti mwazi eza kuti muli poizon tidzimwabe chifukwa kuletsako mukufuna kuti yanu isagwe ngati mukufuna pitani ndinu mukawode zomwe amathila zo mudzipanga ndinu zakumwazo koma ine kundi gwila ndikumwa izi tikhoza kuphana ndagula ndi ndalama zanga wina ango fikila fwe fwe atha kunya manyi seriously apo bi mutsitse ntengo wa fanta afike pakale paja K17 ndetisiya kumwa ngini imeneyi

  67. Ndakuonani,mumakondwa ndikamamwa thobwa pa khrisimisi/nilekelenji ine kukonkha kukhosi Frozy,kodi mwati walakwa Chani?

  68. as I say is country is rich but the people inside into it are weak minded.afailure to to have the heart of making the county malawi good. we are ashamed

  69. Ka gulu ka anthu aka mukumakati MBS nkachibwana, akuloledza anthu kumamwa timowa totchipa tamadzi tikungoulitsidwa chisawawati koma basi busy kumalimbana ndi zinthu zosawopsa ngati izi. Apa zikuchita kuwonekeratu kuti akutumani a SOBo

  70. Oh! What??? No!!! don’t remove happiness on poor malawians!! we are really facing crisis but #FROZY its affordable and readily available,ma products athuwo siabwinoso koma kuDULA eee!!!

  71. Mukathana ndi froyz muthamangitseso maheu aku Zambia. we want our on products koma kusakoma!!!

  72. Frozy is a delicious drink, cheaper n portable, if you want to promote Malawi products, tsitsanii kayee achina fantawo ndi zokumwa zonseeee

  73. Boma losekesa ili, akulimbana ndi frozzy chifukwa palibe vat, osayamba kuletsa achina charger, shooter ndi ma enthanol anzake amene akupha achinyamata ambiri, nanga ndani wafako ndi frozzy,

  74. Osalesa bwanj mowa wa ma sprt upha anthuwu bwanj mwasowa zochita kapena et? Kod kubomako simulesanako mwangokumanako mbuz zokhazokha et?

  75. Why not Dragon, Fusion,Kumbusha drinks, Sobo knows it’s only Frozy cheaper drink and has destroyed their market aash, barman give me frozyyy! ! Jealousy jealousy will kill you! ! Remove all Escom officials if you don’t anything to stop .

    1. Micheal nawo bwanji osachosa msonkho wa fanta,do you know kuti even mafuta ophikira ochoka ku south akulesa,mix kulanda coz ngotchipa than athuwa? They Are charging more tax kuti anthu asiye but still is cheaaper than ours….itts matter of competition basi…ndalama yavuta anthu ayang’ana what they can manage..

    2. Hahaha chaka chino fanta sanasowe….koma iwe frozy….kkkk…fronzy ukadutsa naye boarder mra imalipilitsa ndie manexo xikupita kut….

  76. more than recommended acid in frosy drinks brings health hazards.Test to dip a nail and leave it in there for 2days.

  77. MBS, y today? Frozy anabwera liti mdziko muno? Ngati ndi matenda sitatenga kale apa? Mmene tamumwelamu tikayamba kudwala sukhala mulili? Who is to blame?

    1. The best question must be how many fake materials or foodstuff do we have on Malawi market kodi a MBS iwowa angoonapo Frozzy yekhayu basi?

    2. Ndipo inu zinthu za exp..xili tho ma shop…kumachita kufufutapo…ukadya tastles….koma ndi ndiximumwabetu mpaka alese shooter…black ponda ndi anxake…kkkk

  78. Make Malawi products cheaper. Nearly all products produced in Malawi are very expensive but looking at the country itself, too poor !! Sleeping governments all the times !!

    1. I personally agrees with you, some of us travels a lot and look in Tanzania there more than 200 different types of such drinks and cheaper whilst kunoko almost everything is exorbitant

  79. SOBO lacks innovative concepts to walk in consumer’s shoes. Put away jealous, it starts with our goverment full of failures but resistance in accepting reforms now they just expose their motives having failed to deliver. Leave the poor people alone or do what the majority demands you will avoid criticism

  80. ndikhulupilira kuti sizitheka kuletsa kumwa,kugula ndi kugulitsa frozy.frozy ndi chakumwa chabwino mwinaso kuposa fanta,sobo ndi cola.

  81. Koma bomali latilakwira bwanji?ndidzuwali nkumaletsanso zokumwa,chabwino summer ino mutisiye tizimwa muzletse nthawi yamphepo.

    1. Sobo is a multi-national company. If they run loss definetly they wil close down and take their business somewhere. Now u must know that we are losing investor while we dont have lot of investors in Malawi. Fellow Malawians wil lose jobs. We have lost money that was going to be paid in tax. At the same time Frozy wil come and open legal business and pay tax then take the price up like sobo. So what do u think

    1. Umbuli amalawi udzatipha.”BOMA LACITA BWINO”.Example:tili ndi sobo ku malawi cakumwa cokoma z.Kodi ndi maiko angati akugulitsa sobo wathuyi?,nanga ndi cifukwa ciyani saloledwa mmaiko ena?.AMALAWI MUSAMALOWETSE NDALE PA ZILIZONSE.

Comments are closed.