A Mutharika anangotha nthawi ndi msonkhano wa atolankhani uja – atero otsutsa

Advertisement
Peter Mutharika
Peter Mutharika
Peter Mutharika: Wathiidwa mphepo.

Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika adzudzulidwa mwamphamvu ndi atsogoleri ena otsutsa ati kamba kotayitsa nthawi a Malawi ndi msonkhano wa atolankhani umene anachita lachisanu sabata yatha ku nyumba ya boma mu mzinda wa Lilongwe.

Malingana ndi mtsogoleri otsutsa mu nyumba ya malamulo, a Lazarus Chakwera, a Mutharika anangobweleza zimene anthu akudziwa kale mmalo monena mau a tsopano opeleka chiyembekezo kwa a Malawi.

A Chakwera anapsela mtima a Mutharika ndikuwadzudzula ati kamba kobisa nkhani ya matenda awo amene.

“Iwo asaname, anakhalitsa mu dziko la Amereka chifukwa cha matenda awo osati kuti amagwila ntchito zina zaboma, koma taonani mmene anayichitila nkhani ija. Anangowawula basi,” anadandaula motero a Chakwera.

A Chakwera ananena kuti khalidwe la a Mutharika lobisa matenda ndi limodzi mwa zifukwa zimodzi zimene a Malawi akufunila lamulo lopeza nkhani ku boma lija pa chingelezi akuti ATI bill.

John Chisi
Chisi; Mutharika sanalankhule zomveka.

“Tikanakhala ndi lamulo limeneli ndipo likugwila ntchito yake moyenela, a Malawi sakanavutika chonchi,” anatelo a Chakwera.

Kumbali yawo a John Chisi amene ndi mtsogoleri wa umodzi anadzudzula a Mutharika ati kamba kouza atolankhani kuti ngati akufuna ayimbe munthu mlandu pa kubisa za kumene anali amayenela kuyimba iwo basi.

“Boma si munthu mmodzi iyayi, boma ndi anthu ambiri. Iwo akunena bwanji kuti tiyimbe mlandu iwo wokha. Iwo akuziyetsa ndani kodi?” anatero a Chisi.

A Chisi anati mawu a Mutharika anali oloza ku chipani chimodzi zimene zili zosaloledwa.

A Mutharika adalankhula ndi atolankhani lachisanu patatha masiku asanu iwo atafika mu dziko muno kuchokela ku msonkhano wa UN ku dziko la Amereka.  

Advertisement

182 Comments

  1. A opposition dziwani kt ndinu amene Mukunthandidzila kt dziko lisamayende bwino osati dziko lidziyenda bwino.mukhale patsi mukambilane nokhanokha Muli ndimantha mukuchita kusonyedzelatu kt payi mundale mulibe mutu mwanu koma kusongonedza malo moti mukhale patsi mudzipanga manifesto kt mudzatani kuti muwine 2019. Palibe.Muli.0% a opposition.kkkkkkkkkkkkkk.bola dzanthu.

  2. Ameneo ndiye osusaboma akumalawi. Nthawi yowona kuti boma linapangapo zabwino inapita kalekale munthawi ya Tembo zomwe zasala panozi mdimanyaka a opposition

  3. Amene akuvomelezana ndi president ndi anthu osaganizila mtundu wa amalawi, otsutsa boma akunena zoona, nanga blackout zikukusangalasanitu, ife azanu tatopa nazo. n

  4. zitsilu zotsutsa,mwamulephela petter,komanso akupanani mpaka tizipanitanuto tikutha,munya munthu wake sipetter ndipo 2019akutibulaniso

  5. Mr chakwera ithink ubusa uja was ua best ground not politics cos mfundo zanu zina zikumaveka chitnchalichi siyani pitani muzikalandira zamasika

  6. yankhulan bwino a sam olo atati watula pansi udindo kubwera wina azakhalaso oipa nde mmalawi ameneyo kudziwa kunyoza bas sitizatukuka ata

  7. amafuna tingoona kuti wachila komaso anthu andalewa poyakhula simasowatu pazithu ZOSE amanena kuti adachita ku USA zambri ndibodza lokhalokha ndipo athu amene ali hig grade ya bodza asanamize amalawi anali hospa

  8. Palibe zobakila apa Galu ameneu achingotula pansi utsogoleli palibe cha mzeru akuchita mu dziko mwathu muno Hgologolo ameneyu. mbava .

  9. Pathako Pake Lazaro Chakwera Ndi Chisi Wake Amusiye Mutharika Alamulire Dziko Kod Chakwera Akulephera Kuthetsa Mavuto Ku Mcp Kungokhalira Kutsutsa Zirizonse Basi Ndale Zauchitsiru Akupanga Lazaro.

  10. nonse ndinu zibwete, mwateng dzikongt ndilamakoloanu eti? zachamba bac kukhlila kulongolola ngt ndiakazi koma ndiazibambo, mbuzi zaman kunsi. kkkkkkk mwandkwan.

  11. Akt kumati azawo nkholokolo pano zabwerera mudziwe lake nkholokolozo ndiye kaya azichotsanso bwanji?kkkjkkkkjkkkkkkk ophunzira saposa phunzitsi achina jumbe,chatinkha ndiena otero ndimizwanya pandale sikungoti wakhuta umvekere fwe fwe fwe,onse pano akuthawa amakuyamikira pano aja,amvekere bwana thananawoni nkholokolo zimenezi,court kungolamula pano kuli mziiiiii,tinanena kt fatsani bwana muphunzire ndale ena amatinyoza,ife ndale zapamalawi taziphunzira 22yrs sipano ndikale multiparty abwera

  12. Ngat ukukanika kuendesa bwino chipan iwe chakwera ungaendese dziko iwe?????? Musaone ngat zofuna zamalawi ndizofanana ndizankhosa za assembless ai kt mungazkwanise

  13. The problem is Malawi opposition do not know what to do as opposition. They need to be taught what it means to be an opposition party. It’s very dangerous to leave God and go for earthly things. From church to politics……. Very bad

    1. Nanuso fundo muribe nkharani pasi chakwera anthu ambiri anamuvotera and 2019 apezaso mavote migoromigoro musanimizire zamipinga man tiyenitiyese munthu wamulunguyi

    2. Sizizatheka chakwera kulamupa dziko la malawi God sent chakwera here to win the souls not politics and its very dangerous to a person kugwa mmanja mwa mulungu ndikukayamba ndale

  14. Tembo ánasiyila chitsiru ndye ķu çhurchko unķalarikira chani kumáti man of god ukufuna tate wanga adiwe esheeeeeeeeeeeeeeeeee jusus Christ of nazaret

  15. MCP. Never come back in government mpaka chiweluzo mukanabwele 2004 anayimila agwanda chakuamba.pano zingobwebwetani azanu akudya makobiti

  16. Amazitcha Amalawi Okonda Ziko Pomwe Ali Ansanje Kufuna Ng@ Atalamulira Ndiwowo Koma Sakuziwa Kt Sizingatheke…An2 Akulu Akulu Bt Actng Lyk Small Brainz_iwowo Osapanga Wawo Msonkhano Watola Nkhani Bwanj Mwina Ayankhula Zamutu

  17. Anakutaisani nthawi bwanji popeza Peter Munthalika wa osusa anamwalira koma uyu ndi wa a Malawi omwe anamva zomwe amanena. Inunso mumakamvela zolankhula wakufa munatiuza kuti wafayo. Pamenepo wakufa ndi ndani? Chakwera unalephera ku mpingo walepheranso ndale yang`ana china chochita basi kkkkkkkkkkkkkkk

    1. you don’t understand, that’s why #binwell akuti you have blank heads…….. makani thoooo koma mmutu muli mamina ……. olo mutalimbikira kugwira ntchito. koma ngati ndondomeko za boma zoyendetsera dziko zisali bwino, ambiri amagonabe ndi njala malawi nkumatha zaka 10000 osatukuka…….. just use your brain ……. ukuona ngati ukusangalala ukuvutika……. tiyeni tikaone agogo ako kumudzi ngati zawo zili bwino …….

  18. Mumafuna kuti akuuzeni kuti watula pansi udindo ndipamene mukanaona kuti sanataise nthawi AMALAWI eti? Osamatero tatiyeni nthawi zina tizifuniranako zabwino.

    1. Bertha kut mubwele mzaone banja langa mukhoza kusilira zamavuto izo iwalani the entire family relies on me boma lot ndalama timapanga ndifeyo iwo osazivutikira basi kulephera zamanyazi

  19. Achakwera ndi anzanuwo mukungotukwanidwapotu ulere apa… chonchi ndiye mulowa m’boma in,mfundo zake zimenezi?

  20. whch bible verse says “mucye ubusa mukayambe ndale”??????? wat do u want 4rm our apresident 2 do 4 u …..lets gve hm afull support we ar all malawians & once ur wu cme we gve u also full support czchamba mukuyakhurazi apa “ichi mwakamba ichi mwakamba osaziwa kut znu ziiipa”

  21. zonsezo ife akumuzi tingofuna chmanga chisike bas 12500 yachuluka were falled 2 buy it plz fanz lets talk abaut it

  22. Wanenay Ndan? Lazalo Wauphawi? Hihihi Wayamb Kale Kunjenjemela. Amaona Ngat Amwalira? Wauponda Judax Ndp Ayambe Kufa Lazalo Akhot Akamulamul Kt Apange Covention. Mu2 Umaseka Mchira Wazako Kt Ndwautali Pomwe Wako Wacht Kumangl Nkhata Pamsana?Ukhalir Yoxuxa Yomwey Adzako Tkukhalir Matako

  23. Chakwela Ndi Amzake Akutisokoneza Kobasi, Poyamba They Made Us Belive Kuti Msogoleli Wathu Wathawa, Then anatiuza kuti he is spending our money wherever he is, chomwe chinatikwiyisa kwambili, anapekanso nkhani ina kuti a dad akudwala sali fit kulamula, anazabwelanso kuzati adad atisiya, izi zinatizunguza bongo kwabasi, anatipangisa kuti timuitanise mwachangu, atabwela, anatijambulila mkono waku manja pafupi nationesa kuti mkonowo wafa(we are not even sure if it was really his hand) Kenako Anati Adad Apange Press Comf, Anapanga Timaona Munthu Uja Akuyankhula Mwa M’didi, Akuonesaso Manja Abwinobwino, Pano Nde Akuti Anangotitayisa Nthawi? Chimakhala Chili Chani Kodi? Kusowa Zochita Kapena Kusavala #mwado?

    1. otsutsa akumadya mbanje kwambiri now plz olamula nxt time musazaloreso kuti otsutsa azilima bale bt chimangs coz akaluma mbanje zawozo akumakgalila kusota kufuna kut nafe tifoyire nawo

  24. Kma Yaa, Kukhala Kuja Mwat Wamwalira, ku Bwela Ku Mudzi Osalakhula, Mwa Wapaga Strok, Nde Wayakhula Mwatiso Bwelera Eeah, Ana Ajoka Inu, Panja Mukamulemphela Munthu, Muma Kanyela Pakhomo Kt Aponde, Tsonot Satuluka Mpaka Manyi Anu Auma.

  25. Nkhani ili apa ndi ya Mthalika koma ena mukumba za Chilima Guys zikugwirizana bwanji ? Mulungu akukhululukeni nonse

  26. Mpake mulidi otsutsa, mnsonkhano unachitika lachisanu inu lero ndimukukabwera ndimaganizo amenewa. Inu ndizitsiru zotsutsadi, kuteroku mumafufuza ndalama zomwe zinaonongekatu ndimisala yanuyo. Fatsani anthu azakuvoterani, akakuonani kuti muli ndinzeru koma apo bii mudzakhalira yosavomereza zotsatira zachitsankho kuti akuberani akhakhakha inu zako Chakwera izo.

  27. Otsusa akumalawi samadziwa udindo wawo mwina mukanachotsa mawu oti otsusa muziti othandizira boma mwina akanaziwa udindo wawo.

  28. Ine ndikudzudzula onse include leader of opposition nchito yawo sakuidziwa,Dziko sila peter yekha koma tonse ine problem will face 2gether.Chakwela aganize bwino ali udindo waukulu womuongolera president akalakwitsa osati kumuloza chala sadziwa polakwika

  29. Pamya pawo otsutsao mesa zomwe ankafuna ananva?amafuna atanva zoti nkono wamanja uja wasiya ku gwira nthito?nmafuna munve zot wasiya kupuma n’dalayu eti?????mwanya!!

  30. Ine Nduganiza Kuti, A president Sadataye Nthawi Ndi Press Conference. Osutsa Boma Asaiwale Dala Kuti President Amafotokozera a Malawi Za Ulendo Wake Wa ku Unga, Komanso Kutsutsa Poyera Bodza Lomwe Osutsa Bomawa Anabweretsa Loti President Sakutha Kulankhula wadwalika Pomwe Sizinali Choncho. Bomatu Sayendetsera Pa Press Conference, Dzuka Malawi Dzuka!!

    1. Ambuye…Otsutsa boma akungosusa ndi zoona zomwe. They have been realised to be confusionists because their plans have failed. So no wonder when your hear them with their destructive criticisms!

    1. From 5000 to 12500 ndikuwona kuti monga boma silinaganize bwino ambiri mwayi ife ntchito yanthu ndi yopelekela matope ndiye adatiganizilako sir ,,mukuwona bwaji inu

    2. Samalani ndalama yoperekera matopeyo mukagulile chimanga! Ndipo sichingatsikeso kuposa pamenepa ndie kuti sikumalawi.pompa chakwanila.

    3. Ntengo ogulira uja udaoneseretu kuti chimanga chikwera ntengo. mukawonesesa muona kuti ayikapo 1500 yomwe ikuonaso transportation, packaging, fumigation and other services. mukaona zosezi muona kuti boma silinapange profit yoti nkumakamba izi tikukambazi. koma poti ndife anthu ayi tiyeni tizikambani

    4. Ma corporate company sayendetsedwa kuti azipanga profit koma kuthandiza ma citizens, apopo musinthe maganizidwe anu Gilbert..

  31. Inu nomwe mumakakamiza Mutharika kut achitise mnsonkhano wa a tolankha,lero mukut anangotaisa nthawi?Ndie mumafuna chani apuludzu inu?otsutsa akumalawi amenewo kkkkk zamanyaz ndithu.nchifukwa chake munaba ndalama za ku assembless of God etiii

  32. Koma kaduka ameneyi mufika nae kuti,kod akati kutsutsa ndichoncho? Munya,mukhala choncho ndi nsanje yanuyo agulu inu mixeeew.

Comments are closed.