Mutharika asambwaza Chakwera: Thana kaye ndi mavuto a mu Kongeresi kenako undilangize ine 

Advertisement
Lazarus Chakwera
Peter Mutharika and Lazarus Chakwera
Mutharika (L) wathila mphepo Chakwera (R). (File)

Zimene analankhula mtsogoleri wa chipani cha Kongeresi, a Lazarus Chakwera, pa msonkhano ku Dedza kutha kwa sabata latha zawapezetsa mavuto pamene mtsogoleri wa dziko lino amene naye ali mtsogoleri wa chipani cha DPP, a Peter Mutharika, anaganiza zowayankha lachisanu.

A Mutharika amene amalankhula kwa atolankhani dzulo, anapezelapo mpata oyankha a Chakwera.

“Wina amati nditule pansi udindo wanga, osakonza kaye mavuto ali mchipani chako bwanji usanandiuze ine zimenezo?” anatelo a Mutharika.

A Chakwera anati a Mutharika atule pansi udindo wawo ati kamba dziko lino limakumana ndi mavuto a mnanu kunkhani ya umoyo wa anthu komanso ya zachuma.

Mmene a Chakwera amanena izi ndi kuti a Mutharika asanafike mu dziko muno, ali ku Amereka komwe anthu anatchukitsa kuti akufuna thandizo la mankhwala koma eni ake atsutsa izi dzulo ati ponena kuti iwo samafuna thandizo la mankhwala koma anali pakalikiliki osaka mwayi wa a Malawi.

A Mutharika dzulo anachiona choyenela kuyankha mkulu mzawo a Chakwera.

Advertisement

309 Comments

  1. Amwene tyeni tisiye kulozana zala palibe amene angayendese ziko 100% never olo chakwerayo atakhalapo lero sizingatheke amene ujaso ndye nyanyi,andalewa amangofuna azitipusisa. Komaso muzen chakwerayo kut mulungu anamunyanyala sangaiphule pa malawi pano mcp athu inakwana

  2. Peter mutu wasokonekera Malawi siwa pita muntharika aliyese ali ndi ufulu oyankhulapo za mavuto omwe dziko lathu likukumana nawo not athene kaye ndi mavuto am MCP ,MCP is not malawi

  3. Ithink that’s the duty of opposition leaders to criticize the luring government pamene palakwikwa nde gwape ukukana chan coz this is not abt parties its about the development of our nation.

  4. nanga bwana mutharika akakonze xa kongeresi zitheka? bwana chakwera abakonza kaye za kongeresi kenako mavuto akathako atithandidze kukonza dzikoli ife aDpp

  5. DPP online.Amaona ngat mukuzangothesa chitozo bwana kuiwala kut mulungu simunthu asambwazeni ngakhale zitete ndi mbewa adzidya koma inu mulibe polobulemu mudwale musadwale ine nganganga pambuyo panu monga chokolo chanu hiyaaaaa dpp imandiwaza kkkkk wazaaaaa

  6. Paja ukamayandikira kufa umayamba makani umangoyakhula zopanda mchere awa akalamba let Chakwera atirhandize 2019 chitukuko misewu basi Fotseke

  7. The difference between great thinkers and shallow thinkers, Chakwera criticised Mutharika policies and Mutharika criticised Chakwera on individual basis, who is a great thinker in between the too?

  8. chakwera is not talking about Dpp he is talking about government business he is expressing our worries to u as the head of state malawi needs someone who has a vision and the will of the pipo at heart not bunch of crooks ..

  9. KKKKKK!!
    Mumafuna boma zakuvutani mwayambanso kulira?
    mbuzi iwe eti?
    USALIMBANE NDI MUNTHU MAVUTO ONSEWA NKUMALIMBANA NDI ANTHU? DZANA WANYOZA ZODIAK!
    SUNAYAMBE CHIWEWE KOMA?
    TULA PANSI ZAKUKANIKA UZIKAMWA MANKHWALA UNATENGA KU AMERICA WAMVA?
    USAMATIOPSEZE NAFENSO MALAWI NDI WATHU!

  10. KKKKKK!!
    Mumafuna boma zakuvutani mwayambanso kulira?
    mbuzi iwe eti?
    USALIMBANE NDI MUNTHU MAVUTO ONSEWA NKUMALIMBANA NDI ANTHU? DZANA WANYOZA ZODIAK!
    SUNAYAMBE CHIWEWE KOMA?
    TULA PANSI ZAKUKANIKA UZIKAMWA MANKHWALA UNATENGA KU AMERICA WAMVA?
    USAMATIOPSEZE NAFENSO MALAWI NDI WATHU!

  11. Othawa ntchito yamulungu,amakumana mmavuto adzaoneni ukafuse yona chakwera siunati zazikulu zikubwera nkholokolo umati ukuthana nazo zija sizabwerera ndiye udxionana nazo bwanji kkkkkkkkk usova,kunrna kwandithendithe nanthambwe anazitengera,phokoso litayamba tinane musabwebwete zambiri monga inu busa onani pakhota mukonze kma simunave,kma kuliuza dziko kt mukuthana ndinkholokolo mu mcp,pano zabwerera dziko muliuza chiyani?tinakuuzani mukuphumzira ndale dekhani achina jumbe ndimikhang’a pandale pano ndiizi kaya ine ndingoti dpp woyeeee apm woyeee

  12. Sorry,its Mr Edward Chirwa.I Totally Agree With You Sir.They Shared Our Tractors Among Them Selves.The 3 billion at mera,hw much was spent at UNGA?.its our tax

  13. Kodi ngati munthu akulephera kutsogolera chipani bwino nanga dziko angalitsogolere bwanji? Think twice.chakwera go back to church…

  14. Aaa guys chakwela mulungu anamukwila coz analithawa baible nkukayamba ndale ndee aa tisayembekezele zabwino from chakwela

  15. Let the President without pulling him down.Remember that he too is a human being who happens to be at painly especially when empty tins seem to provoke him.This Homo sapien who fell away from God’s hands should have apologised for what he said after the president’s press conference.He was happy upon hearing the rumour of the President’s health.Let’s be like God fearing pple-wishing each other well.

  16. Peter will not fill shire river with water to reduce blackouts of rain will not come next month believe me expect worse things to happen

  17. Guys sitima imakoma akamayendesa wina, wina aliyense mulungu anampasa mbali monga bwana chakwela, kma lero ayiwala mbali yawo alingat yona kunenevi Nb afune asafune chakwela sangalamulile dziko lamalawi abwelele kuntchito yake

  18. Pa forum yi amene akuikira gvt kumbuyo sakupereka mfundo zogwira mtima zobakira mtsogoleri pomwe a oposition akulemba mfundo ndkuipanga support zomwe zikungosonyezeratu kuti makanni ena ndi opanda nzeru. Osangovomera nkupepesa bwanji kuti sanachitedi bwino….Mxiiiiiiiii!!!!!!

  19. Zithu zangokuvutani musanamizile achakera Inumumat azingosekelera zilizose achakwera zilalakhulani ndithu osaopa akanyimbiwa utsogoleri wabwino amasakha ndichauta osat kuta kulimbira lero zukunyelekanani mukade muthuwana amuthalika amafuna kungotchuka chabe muziona musanat ife ndia malawi sungatipufitse

  20. pajatu muthu akamwa makhwala ambili mutuso sumagwila ndiye achakwera ndi azodiaki amujhululukire nkuluyu ndiwodwala mutuwake sukugwira bwino ndichifukwa chake sonkhano watolakhani anapangitsaso mochedwa

  21. WHY BACKING THE PERSON WHO IS ALWAYS MILKING THE ARLEADY THIN COW…….. If your House is Lit by Escom and Water Supplied Daily Then Say This ….. Tobacco Farmers are Crying,Taxes are Going Up and Being Imposed on Basic Needs,Cashgate Suspects Names Just Sitting On … NDIIYENO NDIKUMASAPOTERA JUST BECAUSE NDI MLOMWE MZANU…… ZA DZIKO NDI ZA DZIKO ….. INSTEAD THE LEADER TO CHANGE HE CANT BECAUSE PALI ZITSIRU ZIMENE ZIMANGOTI INDEEEE BWANA

  22. Mulungu chonde chonde mtengeni mwachangu musogoleli wa Malawiyu kuti mwina nkuwona zina ,mbuye imvani pemphelo langa

  23. Kunod ndkumalaw kungovomeleza tyen tizpangana saport osa kupezelanapo patanyozelapo musamapange ngat mungakwanise bawotu amawona nd amenealikunja.amalawi vuto mchiyani.

  24. Kunod ndkumalaw kungovomeleza tyen tizpangana saport osa kupezelanapo patanyozelapo musamapange ngat mungakwanise bawotu amawona nd amenealikunja.amalawi vuto mchiyani.

  25. U President sichida choopsezera komanso ulingati mvula imatha chilimwe chikabwera.Chonde tisamale poyankhula.Analiko anzanu ankadzitcha amuyaya anagwa chagada.

  26. Malawians
    Its very pathetic kumaomba mmanja kwa munthu Amene akuona anthu Ku mudzi ngati khasu lake.
    Mulungu simunthu dyererani Kaye ,imwani,kondwani ,nyozani koma kumudzi anthu akulira ndi mavuto.
    Fodya 5 cents pa kg mkumati zikuyenda

  27. So many dpp followers are blind visionless people, poverty has ruined their thinking, they have turned inhuman. Blackout, water scarcity, corruption, cashgate are good things to dpp followers? Surely the devil is guieding them but let them know you can only delay justice and truth but a day comes pangavute bwanji when they will be answerable to true Malawians. WHY THESE BLIND FOLLOWERS NOT LEARNT ANYTHING ON CHITSULO CHANJANJES DEATH? They exalted him in 2008 as if he was the one who brought rain for the bummper harvest. They praised him with lots of self exalted names, mose walero, chitsulo cha njanje, mpulumutsi etc. What followed was meant to teach these blind followers a lesson but opss, they turned more blind and started praising this other their leader the same. Believe me and mark my words God will very soon punish you severely unless if you realise no one is super even your so called ndidzakunyenyaninyenyani. GOD IS ALWAYS IN CONTROL

  28. Palibe choyang´ana kwa APM or atabwera OBAMA sangakwanitse mavuto omwe tirinawowa, even BINGU ananena kuti satana anatikhalira pansana panopa ndikuziwona pomwe pastor akusiya kutumikira anthu ake kuyamba kupanga za ndale eishhh zosezi chifukwa chakusitha kwa nyengo u can go to kamuzi damu pano kunawumiratu…… amalawi azanga tiyeni tipephere mosalekeza

  29. Zimatiwawa Ife mbuzi zina zitamadana ndi chilungamo ndi dziko lanji longofuna umvera munthu mmodzi iweyo ndi agogo akowo ndinu mbuzi … Pano dziko lifunika anyamata ….Chakwera akufuna chilungamo chioneke .mchifukwa chiyani anthu madana ndi chulungamo ? Mmandinyasa zedi fotseke agalu

  30. Ine sindingavotere Chakwera. Munthuyu ngwachinyengo. Zoona munthu siya kulalikira nkuyamba kumanyoza anzake? M’busa wachinyengo.

  31. kungobweleza.1,chakwera sanalakwise chfukwa nd mkulu wa otsutsa boma.2,mavuto a mcp siokhuza dzko lose koma chpan cha mcp koma mavuto a pitala nd boma lake nd okhuza dzko lose,a malawi ose akwakhuza ndpo akuva kuwawa zedi.

  32. PEPANI ACHAKWELA MUNGOWAKHULULUKILA MALEMUWA ANGOSOWA POFELA AKUFUNA AZITI ADAYAMBANA NDI ACHAKWELA PRIVETION IS BETTER THAN CURE ASIYENI ADZIFELE,

  33. A visionless leader do not accept advisor, they look at advice as castigation let alone blind political and selfish desire are promoted at the expence of poor Malawians. Poverty has turned many blind and to be educated savages. Learn to run civilized politics. Be a father of everyone not the selected few. We all belong to Malawi

  34. KODI MUKUWONA NGATI MULUNGU AMAKUWONELAN UKONDWA NDI GOGO WANUYO INU A DPP MWAYESA MPANDO WAWU PRESSIDENT UFUMU OTIMUZILOWA PACHIBALE AZANUSO AMAWUFU MPANDO UMENEWU ALA,

  35. Asatinyase Demon Cane wa Ku Malawiyo chabwera Ku manda leave abusa athu alone,mmalo mothokoza Mulungu kuti upumabe muli busy kunyoza anthu,khala phee and c wht God is planining.

    1. Kodi mmaona ngati mulungu wakumwambayu ndiwa Chakwela ekha eti?koma mmadzivuta cos ochakwelao nde mmawaikamotu koma ukanadziwa

  36. Razaroyoso ,sazaununkha Nkomwe Mpandowu Coz Ndotembeleredwa Munthu Sangasiye Kutumikila Mulungu Mkumat Alowe Ndale,nkhan Siyot Akonze Zinthu Koma Dyela Bas Naye Apezu Phindu Eish God Lamuliran Nokha Zikoli.

  37. Peter alibe chonena kambani zamavuto muthanawo bwanji koma basi nkumalimbana ndi ma Radio kenaka achakwela hahahaha ulamulilo wavuta yapa

  38. Kummwera Kuli Maboma 14 Kuli Anthu Ambiri,pakati Maboma 9 kokanganilana ndi dpp chifukwa alomwe ali paliponse,ku mpoto 6 Koma Amakwera Yolamula.Achakwera Dpp Imawinira Kummwera Chifukwa Simuingawine,ndipo Mpovuta Kugwetsa Boma Lolamula,taona Anthu Onse A Mcp Akuukilan,mwasala Nokha,munalowa Field Yolakwika Is Better Baibulo Lomwe Lija.

  39. Mmalo moti awuwudze mtundu wa MALAWI zomwe amachedwera kuti apinduranji osanena zimenezo ayi Koma kulimbana ndi Achakwera zadziiiiii .Bwanji osamangomwa mtera atenga Ku UNGA!!!!!!!!!

  40. Munthu wanzeru sangasiye kutsogolera nkhosa za ambuye ndikuyamba za ndale Mulungu wakwiya ndinkona zao zisakuyenda

  41. kumusakaniza ambuye amakana. bweleran mukakbweze nkhosa mukhola lake zikusochela chifukwa mb’usa kulibe ali buzy kuchipani .

  42. Ndiye kuti peter ali bzy kukhoza mavuto aku chipani cha achimwene awocho kenako za dziko mmmh ndiye liti ?.Misonkho ya anthu osauka ngati malawi kukazikhalira kunja mpana mwezi ,awononga zingati?Esh my Malawi.Apeter chisoni mulibe mukapita kumidzi ndikukawona anthu omwe mukwaberawo kuonda kwake anthu odya chauya ,therere Kkkk

  43. Koma chimene ndimadziwa ine chipani chikakhala ku Opposition ndi ku ma nyozedwa pafupipafupi chipanicho chimawina eg PP vs DPP! kkkk!

  44. sibwino kuti amalawi mukwanyanya waumphawi chifukwa chakuti anthu odziwa akuba,abodza akukanika kufufuza anthu aja adaba ndarama za amalawi osawuka aja ndiye umkumayima apa umkumayikirana kumbuyo muwasi amarawi arankhure mwawufuru wawo

  45. Wanena zomwe wawona osati kusambwadza musamabweletse zigawano kuzipan ndinu makape mw 24 mulungu aliko zonyozeka zalelo mawa zimapatsidwa ulemu ilindidziko peter munthalika chakwela amalankhulila ifeamalawi telo sadaziyikem’mavuto komaso ku MCP kulibe mavuto m’tsinje umalimba m’ziyangoyango bless chakwela our god

  46. koma mwati a chakwerawa ndi abusa?abusa ake a satana kapena a mulungu.Koma baibulo alinawo?nanga ndale amadzidziwa?kodi iwo atatenga dziko lero palibe chomwe anthu angadandaule?ndi dzikotu ili.Mulungu sakondwera ndi makhalidwe otere.Adikire 2019 ndiye azayambe campaign.

  47. Koma ndiye munthu odwala odwala. kumvetsa chisoni kwambili munthu ameneyu kungowononga wononga dziko lathu?? kkkkk koma abale akuti prophessor, uprophessor wake wa using’angatu. kadziko kakang’ono kukakanika kukalamulila.

    1. IWE PAMTUMBO, KUKANIKA KULEMBA NDANI NGATI UKUKOMENTA SIKUSONYEZA ZOTI WAMVA GALU IWE WACHABE CHABE. IWE IFE TINAVUTIKA NTHAWI YA KAMUNZU PALISO CHIYANI APA TINGACHITE NJENJENJE ZA ZIII. LELO MALAWI ALI PA NUMBER ONE UMPHAWI PADZIKO LOSE LA PASI NDIKUMATI NDINE PROPHESSOR.

  48. Chakwera sanalakwise iwe bwapini pitala mavuto amene alimuziko muno sungayelekeze ndimavuto a MCP popeza iwe bwapini wanyamura anthu 17 milion muziko muno frishiiiiii Mr ibu kuyakhula kopanda zeru mcp mavuto Ali muchipani chawo nanga iwe mavuto muziko muno uthesa liti bwapini kupusa basi chiwone kukula muto ngati bakayawo zeru chilibe magesi akuvuta mazi akuvutaso muno mziko njala anthu ndiposo kwacha akupitilira kugwa phavu ndimavuto womwe umawalonjeza anthu pathawi yakapeni kuti uzathesa malata unasisa komso cement komso ndunazako Aruba ndalama chaponda khope ngati tmbo hule kaliati wose awa alinimavuto muwulamuro wako bwapini frishiiiiii

    1. Kmtu kunyoza kumeneku olo mutamutukwana chotani mpando umeneu simuzaukhalila pamoyo wanu onse bwezi mukumangokhoza mtima wanuwo kt yesu akazabwera ndiza khalila mpando wake uti?izi nzadziko lapasi zosala tizingolipepherera dziko lathuli kt mulungu aziliyendesa bwino basi

    2. Ine ndine wolimbikira agalu inu simungalimbene ndi ine mbewa inu or ine sindimavota chifukwa agalu andele angonamiza chabe anthu ndawonera bwapini woyamba ndi wose agalu a Dpp ndi lhomwe people frishiiiiii nose agalu inu

    3. ,@ muwamba point of correction ….sikuti athese mavuto akunyumba kwa munthu ayii koma mavuto omwe wabweresa iye u can’t see if ur naked maso

    4. Onse ndi mbuzi za anthu za muchombo konyera. Dziko laonongeka basi nyo nyo nyoo pa msata basi amupase bushiri mpando kkkkkk

  49. Anthu enanu ndinu omvetsa chisoni ndithu, muzitha kutsiyanitsa zinthuzi, mabvuto achipani ndiwokhuza anthu ochepa koma apapa achakwera akuimira kulangiza pazamavuto omwe akukhuza dziko lonse la malawi koma winawe ndi agogo akowo nkumati asakulangize popeza iyenso ali ndi mavuto. Nonsense!….ndisiye ndiziononga poti iwenso ukuononga…is that how malawi of today gonna be? Tingatukuke koma? Pali democracy apa? Kaya ine dziko ili silizatheka ndi atsogoleri otere

    1. Komadi ndizoona mavuto amuchipani amakhuza anthu ochepa ndipo monga akhuzila anthu ochepa mposavutanso kuwatjesa, koma chakwela akukanika kuthananao ndiye tingoelekeza kuti amupasa usogoleli wamalawi tonse ndiye angakwanise? wanzelu opanda mamina mutu mwake atha kuvomeleza kuti sangakwanise kusogolela dziko ndipo akuyenela asove kaye mavuto ake

    2. mwandsangalatsa man, 1,chakwela nd tchto yake ngat mkulu wa otsutsa.2, mavuto a mcp si a dzko lose kma achpan kma mavuto a peter nd boma lake nd adzko lose.

    3. Adalephera kuyendetsa mpingo ndiye angwanitse dziko? Akulephera kuyendetsa chipani ndiye angakwanitse boma? Munthuyu adazolowera kungolandira satha kugwira ntchito. Munthu wamanja lende. Kuyendetsa boma ndi serious business.

    4. Kkkkkkkkkkk koma nkhaniyi ndiyosekesa coz omwe anavotera Dpp ndiambiri koma omwe sanaivotere ndiochepa example Mcp, ndiye mukamati Chakwera akuyankhulira aMalawi onse ili ndi bodza coz anthu ena amumvesa kale president inu a Mcp zisusani mpaka yesu kubwera bolanso John Tembo

    5. Ndakunyadilani amalawi anzanga nonse, maka amene mukutsutsana nane, chinthu chimodzi chomwe tingakumbutsane mwina enanu simukukumbukira, mpovuta kutsutsa mtsogoleri wadziko than wachipani chabe, pulezident amalemekezeka kwambiri kusiyani ndimsogoleri wotsutsa…izi zilichoncho kamba koti chilichonse pulezident timampangira ndife tomwe monga ma citizen…ndalama zathu zomwe ‘ misonkho yathuyi’ ndizomwe akunjoya nazo, pomwe iweyo mnzangawe ndi ine ndemwe…lero tikunena pano, wagula candle koma mnyumbamo magetsi angochita kuzima, madzi amene ukumatunga utsiku nkusunga popeza mawa kulibe, bizness kulibe umapanga zometa magetsi kulibe ana ako akuvutika, kuchipatala akuti mankhwala mukagule ku pharmacy koma iwe ndalama uyitenga kuti sunatsegule shop kamba kamagetsi, njala yilinso mkati Mmm tikamawombela mmanja tizidziwa zoti mwina si ife… Zathu zilibwino koma azakhale ako, azichimwene, ankolo, azichemwali kumudziko zawakhuzatu,… Iwe wandale wongowombera mmanja zilizonsewe…lingalira bwinotu, k1000 ungafupidwe lero siyingakwanetu kugula zosamalira banja lako, koma nkumatsekelera …asaaah nyasiii!

    6. Zomwe ukunenazo zikusonyeza momwe iwe ulili, it means ur head is so empty…umangokankhidwa like an empty vessel kkk mwinanso kuchipaniko ndiwe woimba ngoma…ha ha ha

    7. Chipeta , chikhala Malawi ali ndi anthu oganiza ngati inu bwezi zinthu zikuyenda bwino koma vuto kunuachuluka mbuli zosakmganiza bwino zoti akazipasa K1000 nkuiwala mavuto awo ose. Monga anzathu akumwera kkkkk eish nimavuto kwambiri.

    8. If you remember very well the opposition leader said the president must resign.Imagine the president resigned today is this going to address all the challenges malawi is facing?To my opinion i thought the opposition would hv come with the solution to proove they are capable of solving the challenges.Through your own means you would hv contributed in reducing the scarecity of medicine in our hospitals,how many opposition parties here in malawi did this,not even one.I therefore think that be opposition is not to make others failures ..be part of the contributor to the nation.if you realy love your nation and part of the citizens of mw learn to take part in developing the nation.You find that some pple might be part of tax invassion people for example with an intention of making someone fail and yet the ones who need medicines in hospitals are our nephews and aunts.lets be patriotic

  50. kwa amene zukuyenderani ndimwai wanu koma ngat ena sizikuyenda simungawaletse kulankhula mogwrizana ndimavuto awo chakwera status yake is improving koma sangakhale chete ena zkuwavuta chifukwa cha leadership yope iripo

  51. 577bn dpp cashgate,MSB illegally sold by dpp,Tractors stolen by dpp,15bn cashgate at agriculture under peters watch, 3bn at MERA under peters watch, News of corruption ,Frauds is the order of the day in Dpp regime.How much was spent on UNGA trip ? How many did he take to UNGA ? Last year it was the whole village .This is Tax payers money malawians deserve to know.577 bn dpp cashgate would have bought power from mozambique,and buy drugs.Thieves at work.

    1. we wouldn’t have even borrowed money from the chinise government for the stadium n BICC we could have used our own resources to build these facilities komaa dyera enao mpaka ma tractor kushopetsa iiih

  52. mayazi sizoti achakwera mwakut kwakutizo apa,to me sanalakwitse coz ndi mtchto yake ngt otsutsa amayenera kulankhulapo pazomwe nawo ngt otsutsatu ndati aona kut akhoza kuyankha,that’s the power of democracy,,,big up ochakwera msafooke angatambalale anthuwa ndi misonkho yathu imeneyo

  53. Olo lero Peter atangoti watula pansi udindo a Lazarus Chakwera simungaunukhe udindo umenewu you are too far chifukwa a Tembo anakusiyirani ndale anadziwa palibe chabwino chatsala Ku MCP,Tembo sangangosiya zithu paulere anaionera meter patali.

    1. Muuzeni mbuyanuyo akonzemavuto tili nawowa rather than kumalimbana ndi Chakwera. Stupid comment. Muuzeni tatopa naye. Nyamakazi mpaka one month ali ku USA. Ngati ali wanzeru alikonze dzikoli osati za zii tikuonazi

    2. alomwe ndiamenewo mbuli zawathu. Okuti chimanga tizigula mk250 profesala ameneyo walomwe heede mubeso 2019 mwayi mchilima wanuyo muyaluka

  54. Palibe chanzeru kumuyankha Chakwera ndikuwawidwa ntima chabe koma mavuto ku dpp ndiye alibwee ngati simukudziwa dziwani mmayesa ine konko akudilira mpando wakewo akuti ndi achinyamata bola kukongelesi anthu akudziwa kuti ndizotumidwa koma simuitha kongelesi chitha ndi chipani chanucho Udf inkatani lero sifwaa basi nanga .tsogoleri wake alikuti?

  55. the boss on the move,,,_____atsala awa a Malawi24 akusambwadzeninso…..Dont take peters quietness as a weakness…..//mumva kuwawa

  56. Amayetsa ngati, ali m’tchalichi kuti anthu anena Amen. Chakwera mbuzi yamunthu kwabasi, sunafike polangiza president iwe ubwere kwa azibusa anzako akakumvera. Uku wayambaku, ngakhale utamufunsa John Zenus Ungapake (JZU) Tembo akuuza bwino zampando umenewo sikwamasewera ayi.

    1. Man boma silimazatitenga ife mwamva,,,,,ndipo ndalama zomwe zimathandiza kutenga anthu ku Joz si za Mr IbU,,,,ndalama zija ndizathu Anamuika pa Mupando ndanie?si ife tomweee,,,, simunati mukhaula ndima black out.

    2. Malawi ndi kundende yoyendera koma eni amalawi saziwa. Mavuto onse ali mmalawiwa pali chosapotwra apa?. Taziyendani maiko anzanu nkumaona osati zoola zili mmalawizi.Inu nkumaonda koma yes bwana osasiya. Ena or aphunzire bwino koma mmitu mwao ndi thonje basi. Umati osusa boma azitani ndipo ndi udindo wawo kutero osati zambwererazo. Simungazimvere chisoni magesi, madzi, katangale ,njala ndi zina pomwe mukusapotayo zonsezi sizikunkuza. Ukauzolowera umphawi sibwino kulowerera kupanga kommenti zinthu zokhuza dziko. Pali za chipani ife we dont care ndiye pali za dziko ndipo ndi ndalama yathu imene akumatizuzirayo.palibe zonamixana apa or RAS Zuma amamuuza poyera chifukwa anthu safuna kuswa msabwe dziko lokhala lawo. Joice Banda anali wamkazi koma no black out. Why Malawi ??!!!

    1. Munthu Ovetsa Chisoni Iwe Busy Kunyoza Azako Iweyo Ndi Pitala Wakoyo Pamaso Kuphwanthika Ngati Vampire. Nyawu Ndi Ndani Basi Kuzolowela Kutenga Madzi A Mkapu Kukathila Kunyanja Mbuzi!

    2. mukumvabe kuwawa peter anakalamulirabe mpaka 2019 mumaona ngati afa akakhala chakwera wanuyo wothawa mpingowo akalambira ku opposition konko akafunse tembo

    3. Nose okongelesi mulutaya thawi nunyoza pitala ichakwela oyona tsanu okumana nimafunde panyanja nameo muluwaona mavuto yosatha mchipani

  57. zikuwavuta kuyendesa cipani ndipo liu la loti achoke liri mkamwa mwa achipani nanga dziko angalikwanise?auzeni achose chimtengo mdiso lawo kenaka aone chaamzao zikawakanika akapepese ku chihema

  58. Munthu osamva uyu,ndimayesa chakwera amafuna kumnthandiza koma kusayamika madara awa.Ndiye blackout,kwacha kugwa mphamvu,madzi ,kukwera kwazinthu ukudikira chakwera athane ndi mavuto amchipani chake ndipo uzakhoza mavuto alipo awa.Wake up mr A.p.m

  59. Pamenepo wanena zoona chotsa chitsotso chomwe chili mudiso mwako then ukachotse chamzako , chikwara amaonjeza

  60. Please chonde tazingomwa ma tablet otsalimbana ndi anyamata paja yangosala matsiku wowerengeka eti,,,,Chakwera otsamtengera munthu wodwalayu ndi matenda akufuna azibale ake azikanena iweyo ndi amene wamupha.

    1. U fool why don’t u shut de fuck up ..believe u me chakwela will Neva rule this country..mgalatiya opusa iwe ..amene amwalila kunyanjawo akuuza kuti anali adwala…wina aliyese akhoza kufa . including ur chakwera who escaped God calls..stupid galatians…fool

    2. Usandikumbuse nthawi ya MCP Uncle anga ali pa Chanco anamangidwa ndiye za Chakwera zanuzo ine ayi ayi ayi ndikutitu ine ayi abale funani wina and by de way who iz Chakwera?

    3. Koma mchele ukuthatu chaka chino agalu inu fweeee ngati anakulozan bwampiniyo #moron iwe P Dalitso undisamale wamva ndikuchosa mano amene asalawo

  61. yes peter is right , first chakwera must solve the problems in his party mcp ,then give advice to the president, ungachotse bwanji chitsotso cha mdiso la mzako ,chako chili mdiso lako?

  62. kodi achakwera angalamulire dziko chomwe amafuna munthu nkulawa mpando umenewu osati kutsogolera bwino chili kwa nzako chigwire nyanga koma tagwira iwe nyangayo kulephera achakwera ngomvetsa chisoni osangokhala bwanji kungomva kuti ngotsutsa adzingotsutsa chilichonse

  63. Anthu awa amadziwana poti amadyera limodzi i lyk dis song by Evance meleka,nde pagona ndalepo nde pamenepo,ps ndale palibe kunens chilungamo.

  64. Amalawi ndiye muli pamavuto atsogoleli mbuli owatsatila mbuli nose ………. Ife pa theba pheee kuonelera ku Malawi uchitsilu wa utsogoleri

    1. Palibenso cha mzeru. Let him show us amene amakumana nawo ku USA. We have told this several times but the only fruit is retrenchment

    2. He is just the employee , just like any civil servant , nt the President , koma Bingu he was more than a President

Comments are closed.