A Mutharika mwina ayankhula kwa a Malawi lero

Advertisement
Peter Mutharika

Pataphulika mphekesera zoti mtsogoleri wa dziko lino anachedwa mu dziko la Amereka kamba koti anagonekedwa ku chipatala, mkuluyu ali ndi mwai otsitsa nkhani zimenezo lero mwa yekha.

Malingana ndi a kunyumba ya boma ku Lilongwe, mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika lero akhala akuyankhula ndi atolankhani.

A kunyumba ya boma ati a Mutharika alankhulana ndi a tolankhani lero zokhudza ulendo wake wa ku Amereka koamnso nkhani zina.

A kunyumba yaboma ati atolankhani oposera makumi anayi aonetsa kale chidwi chofuna kumva mtsogoleri wa dziko lino.

“A President akumana ndi atolankhani lachisanu, pa 21 Okotoba,” anatero mneneri wa a President a Mgeme Kalirani.

Anthu ambiri akhla tcheru kumva a Mutharika kamba koti atafika mdziko muno sanalankhulepo ngakhale liwu limodzi ndipo anli okanika kugwiritsa ntchito mkono wawo wa dzanja lamanja.

Atafika anthu amene anali ndi chikayiko kuti mdziko la Amereka mkuluyu amadwala, anavomeleza ataona mmene anakanikila kugwilitsa ntchito mkono wa kumanja.

Advertisement

134 Comments

  1. chilungamo chake athu akumipandowo akuchidziwa, sangawulule. koma pot ndimatenda bisan akanakhala maliro akadanena’

  2. KOMASO IFE AMALAWI NDIFE OMVETSA CHISONI KWAMBILI. PRESIDENT ALIYESE AKAMAYENDA KUPITA KUDZIKO LINA AMAKHALA NDI LIMIT. IWOWA CHIMENE WATHELA MWENZI KUMSONKHANO WA UN OMWE UNALI WA MASIKU ATATU OKHA CHIYANI?? KOMASO MPHEKESELA ZA KUDWALA NDIKUFA KUKUNENEDWAKO SIKUNAYAMBILE KUMVEKA KU MA REDIO STATION AKUMALAWI KOMA KUNJA KWA DZIKO BWANJI OSALIMBANA NDI ANTHU AKUNJAWO BWANJI??

  3. Nkhan imeneyo yundinyasa kwambili kaya akudwala kaya sakudwala azidziwa yekha mukubisa matenda chinachake chikachitika tidzava.

  4. Kkkkkkkkkkkk ptar akumana nazo relo matenda mbali akathana akutikomweko ndi soja.lusiyasi banda ndiposo wadelela akutiso sakuopa anaziyambila kalekale thaw ya kamuzu ngati anamulephela akuakulu thaw imeneyo Nde unyundendani. ..bajatu musamuiwale lusias amafusa pakana muthu yemwe akumufusayo pakana kumwalilandi Bp ndinafuso

  5. madala. Mwavelanokho ana anuwa akukhalangati akukunyozani km ayisichocho kukudandawulila ndimene dzikolathu likuyendala. Chonde tayesesani kubwelapoyela ndikuwuza thundu waamalawi chowonachenicheni titsana madala zikowathuyu akupiti kuphophotsono likukhalangati lilibetsogoleli OK km ndilindichikhulupililo kut kulilakwathumwakuve ndithu ndikuziwakuti muchitapokathu

  6. Kodi sanali pa wailesi? Chifukwa atola nkhani amanama kwabasi.
    Anatiuza kuti Peter wafa, lero akukanira anthu kuti inali mphekesera ua m’chipatala. Anthu ake ati oposa atola nkhani?

  7. umbuli ndiumene ukutipha kodi mene munayambila kunyoza munja mwapindula chani agaru inu eeeee tamusieni muthu azipuna zake zinayeratu inu mukhalila yomweo yomanyozayo eeee alesi

  8. Amalawi dziwani kut boma lakangalika kupanga ma reformz so,,,kusowa kwa mankhwala + ndalama,,,kuvuta kwa magetsi + madzi & kukwela kwa mitengo ya katundu + kuchedwa kwa malipiro ndizipatso za”public reformz”

  9. From where I’m seating. ..it is 1:15pm. The count down continues. In 45 minutes I want to see my president speaking to journalists in robust health. I guess I will see him gesturing using his right hand and not his left only.

  10. Abwana awuzeni anthu kuti mukudwala,chifukwatu ndizochita kuwonekelatu nanga muzichita kubisa ngati mutodwala kanyela isiii!!!!

  11. Koma muli ndi mbiri vuto lanu chenicheni ndichani yoh yoh pangani zanu zimene zingakuthandizeni.mukulimbana ndi munthu woti ali ndi ndalama kale zake zinayera kale inu koma kukanda akalungu nsense.kunali muluzi analipo enaso ena amalimbana naye chifukwa chakuchita bwino kwake pano muluzi ali kuti????? Samalani abale polimbana ndi anthu andalama muzafa imfa yowawa

  12. komaso kuti mufuna a malawi tiziyendela yiti pakuti kamuzu amatichuma chilinthaka muluzi amati changu anyamata pa twon Bingu amati amalawifesiwosauka tiyendepamodzi ndimtimawumodzi amayi amati amayitakatani nangayinuyo muwuzathunduwa malawikutichani azingoyenda popandatsogoleli tatiwuzani

  13. Ayankhule kaya asayankhule ndi ufulu wake mukulimbana ndi munthu oti atamwalira inu simungapasidwe mkhale spoon yake tiyeni amalawi tipeze zochita not kunena munthu oti zake zinayera kale mphindu palibe ngati adwala adwale iyenso ndi munthu

    1. Koma mwaimvesesa nkhaniyi? sakunenakuti ndichibale komamonga tate wazikolino yemwe akudyelela ndalama za misonkhoyathu akuyenera kutiuza kuti adalikuti?ndipo amataniko akalongosol mpamene ifetiziwe chilungamo so usaakhomelele atolankhani pamozi ndi amalawi onse amene alichelu ndikhani yokhuzana ndi tatewathuyu thanx

    2. Muha inetu si mphawi ngati iweyo omayang’ana zamwamba kukacha,mbuzi ukunenayo utha kukhala iweyo ndipo yeniyeni ndithu mwina sukumuziwa yemwe ukukamba nayeyo,usamale

  14. Atolankhani please Kandifunsireni kwa a president wo kuti “Malinga ndi kasololedwe ka anthu m’bomamu kapangisa kuti anthu akhale pa umphawi wa zaoneni, Monga kukwera kwa zinthu, Kusowa kwa mankhwala ndi zipangizo zina muzipatala, Njala, kuzima kwa magesi , Kuchedwa kwa malipiro, Kuchepa kwa chitetezo, ndi zina zotelo, Inuyo simukuchitapo kanthu mungoti phe.Kodi kuti inuyo mutulepansi udindo wu ndikupatsa munthuoyenera ndikuti muzilamulabe koma anthu azikoli azizunzikabe Çhabwino ndi chiani?”

  15. Amalawi24 zining.a siza bho best way mphekesela zoti ntsogoleli wa dziko lino wa mwalila ifeso kuno kuti tidziwe zoti wa mwalila tina ona inu muta panga post yoti watisiya osati wa chedwa kwa merika

  16. kodi chifukwa chiyani anthu mumamfunila nzanu zoipa??? u like or not but president Peter Mutharika ndi mtsogoleri wa wanu.apresident akululukileni anawa sadziwa chomwe akuchita

    1. Ngankhale ali ana komandiamene anakavota kut iyeyompaka akhale wamkulu. ndelero akamayankhula musamawakanizeni ayi coz voteyao ndi imeneikulakhula palibechimene angayankhure iwepamenepa adha inu

    2. koma olo muphuphephupe iye ndi mtsogoleri wa dziko la malawi. olo upite ku maiko a kunja kukufunsa kuti mtsogoleri wa dziko la malawi ndindani umutchula ufune usafune…and palibe munthu amene amanfunila nzake zoipa pamatenda iye ndi munthu olengedwa ndi mulungu ngati inu. kukhala president dsnt means kuti sangadwale or kumwalira

  17. A malawi 24 ndinu mbuzi kwambiri lero mkuti ali ndi mwai wosusa zomwe zinkayankhulidwa nthawi yomwe anali ku amereka . Mesa mnkati anamwalira ndiye lero asusa bwanji coz anamwalira ?

  18. Kaya Ine ndkuyika 4n yanga pa Solar coz magasi anaonongeka kalekale kenako ndkukatunga madz ku mjigo ammatap anafa kalekale,, Nyasaland wanga iwe kod ukulowera kutko?

  19. What ashame to malawis selfish, heartless, insensitive politicians who reguard malawians as fools. Denying an issue which can even be noticed by cats & chickens. Shame!!

  20. Malawi 24 tomorow dont change subject. Mwatiuza kuti President amadwala. Kodi simukuopa kunjatidwa popeza enafe ufulu wolankhula anatilanda akamuna. But why this hide and seek game. Kodi matendawo ndiopangitsa manyazi?

    1. U got it wrong. They said rumours and they have posted it. Which means they have evidence. And if u read the post 4rm yesterday. They posted that anyone who post sickness of the president wil be arrested. I dont understand yo corncen here. To be sick or not doesnt matter to me. All we need to know is the truth. And as a matter of fact i have freedom of expression unlike u. And my rights have to be respected, like it or not i wil remain the same. Do u want me to comment what u want and what makes u happy? Ahah this is a free democratic country, yo views are not my views. U have a right to urgue with yo opinion not to imidate my opinion. I think at some stage i must fund a civic education so that u wil understand yo rights and how to pratice them correctly without violating other pples rights.

  21. Komanso tazionera tokha akugwiritsa ntchito dzanja la kumanzere zomwe sanapangepo mmbuyo monsemu, kukanika kukwera Galimoto, kukanika kuyankhula nafe nthawi yomuchingamira ndiye azisutsapo chani? Kodi matenda/kudwala ndichinthu chochititsa manyazi?

    1. kudwala sichi2 chochitisa manyazi koma anthu amatengerapo mwayi kuchita zomwe amadziwapo akakhala kuti muthuyo amadana naye (sikuti ndikumuikila kumbuyo presidentyu ayi)

    2. Iri ndiro bodza kodi.munthu tingamusenkhe yemweyo ndikumamuda nde chani? m’gwede gwede oseu wabwela bcoz boma likubisa ndi boma lamutenga peter ngat m’tsogoleri wachipani basi. koma zoti peter ndi tate ot adasankhidwa ndi anthu sakudziwa.ine ngati zika voti yanga ndiimodzi yomwe idachititsa kt peter akhale presdent nde ndilephele kudziwa momwe munthu yemwe ndidamuvotera alili?

    3. amwene a Bannet munthu wavomera momveka bwino pa press briefing yake kuti amadwala ndipo vuto la nkono wakumanja mukunenawo wafotokoza

    4. Press briefn yake itii mesa anakana kma wat nyamakaz ndyomwe umamuvita nde anamupanga inject Jackson wanyamakaz ndemkonowo unapanga namu kkkkk

  22. Peter ndchixiru kwambri ..y angovomeleza zot iyeyo amadwala??? Iyaa…it’s better angomwalira bax coz tatopa naye guluyu.. Akagwere

  23. Chimene ndimadziwa ndichoti President amapangisa msonkhano wa atolankhani nthawi yomwe akangosika ndege ku airport ndiye izi ndiza chilendo hahahaha lol

    1. sindimayesa ndi fb yomweyi imalengeza kumwalira kwa nkulu yu koma atolla makani enanu ndi odabwitsa zedi kumene mupita mukafunse bwino za kumwalirako chifukwa munaphatu wachikulire nthawi isanakwane

  24. Alankhula lero tikukumva kuti ati chiyani amati akudwala mwakayakaya.Ena kumakamba zakundata tione lero Mtsogoleri waMalawi akuti chiyani

Comments are closed.