Hule amugamula kuti akagwire ukaidi zaka ziwiri atatentha nyumba ya kasitomala wake

Advertisement

Khoti laling’ono la Chisenjere mu mzinda wa Blantyre lagamula mayi wina oyendayenda kuti akagwile ukaidi wa zaka ziwiri atapezeka olakwa pa mlandu otentha nyumba ya bambo wina.

Khotili linamva kuti mayiyu, wa zaka makumi awiri ndi mphambu imodzi (21) anatentha nyumba ya bambo wina, bamboyu atalephera kumulipira iye atamusangalatsa.

sex-workersKhotili linamva kuti pa 27 Sepitambala chaka chino, mmayiyu amene dzina lake ndi Ellen James amamwa mowa limodzi ndi bambo wina pa malo ena otchedwa Soul City mu dera la Chileka.

Akuti awiriwa atamwa mowa anazindikira kuti akukondana ndipo anaganiza zopititsa chikondi chawo patali. Iwo anakachita za chisembwere ndipo atamaliza bamboyo anakanika kulipila. Iye anapempha kuti azalipile mtsogolo.

Akuti mayi oyendayendayo anamuvomela koma bamboyo anayamba u kavuwevuwe ndi kumangozemba ndi ndalama ya mayiyo.

A James pokupsa mtima ati anakatentha nyumba ya bamboyo ndi kuononga katundu okwanila K400,000.00.

Poweluza mulandu umenewu, oweluza anawalamula mayi James kuti akakhale kundende kwa zaka ziwiri ati chifukwa chotentha nyumba.

A James amachokela ku Balaka, mmudzi mwa a Matola. Bambo amene wawapititsa ku ndende uyu, a Polisi akana kumuulula ku gulu.  

Advertisement

101 Comments

  1. Kodi nkuruyo saripabanja? nanga nkazi wake aribe bwetete? ndisachedwe ndimafuso apa chigamuro changa ndiichi bambo iwe m’chira wako hure kundendeko mzimu wako uwuse muntendere kkkkkkk?

  2. If interested all cute ladies available in this group who needs a guy to give them good sex and this includes all sugar mummies or just older ladies but should be smart and ready to spoil with money inbox or call on 0882926882 same line hit me on whatsapp, love you

  3. Haaaaaaaaaaaaa kkkkkkkkkkkkkk koma inu inu ohooo zosakhala bwino ma guys tiyeni tizikwanilisa zomwe tagwilizana osamango chinda amkaziwa mulibe cash njala yathuyi simuyiona nanutso amakhoti samakondela pogamula mlandu mdalayutu nanaye ndiolakwa akanapeleka dollar zikanathela kumjangokoko izi ndipo sitikanaziziwa izi ok

  4. koma azimayiwa akuonjeza. tangoganizani mnthuy mwnanso anamupasanso zokandakand ndy kumuotcheranso nyumbA? aaaaa! two yrs yachepa kwambr

  5. hule ndimamuna aliyese wachilendo amalandiliratu ndalama koma m’mene ndikuvera apa kusonyeza kuti anali kasitomala amavesesana amatha kumukwera pa ngongole..koma chomwe chinavuta bambo ameneyi zikuoneka anajaira anayamba kumutenga hule ngati chibwez chake kuti azimukwera ulele asanakambilane ndi huleyo..pomwe hule sazaloweleka alibe zoti wamukwera nthawi yayitali wakhala ukumulipira umayenera ulipire basi..pokhapokha mwina ngati amakufila iyeyo zimatheka kumakuitana ulele mwinaso kupita ku room yake kukutulutsila ndalama zomwe wakweletsa tsiku limenelo kukugaira zina mpaka kutenga kukamwera mowa ndiiweyo…kwaine ndikuona bamboyu ndiye olakwa ali ndi vuto amafuna kumaonetsa ushasha kwa hule pomwe hule safuna uzimuonetsera ushasha

  6. Malonda opanda oda.mahule ena amachita kudzitama akuti ali ndi zokoma (kadya ubwelere) aliso ndi ma style awo step iliyose ili ndi kam’tengo kake.utafuna ugone pompho ADMIT koma ya prain pakatipa inakwela inafika 5pin.koma panopo chifukwa chakugwa mphava ya kwacha zatsikako ma 2.5 pena ma 2

  7. Zili bwino chibwana chimakanda opusa, wina kundende pamene wina nyumba katundu zidapsya, ulangidwilatu pasi pompano muyambepo kumdziwa mulungu muluona bwa!!!

  8. Ndie mukuti hule wamangidwa chifukwa chotentha nyumba ya bambo wina? Hule wamangidwa chifukwa chotentha nyumba ya hule mzake, period. Mwamunayonso ndi galu wa munthu, osangokwatira bwanji???

  9. Mayi siwo lakwa olakwa ndi bambo yo kodi mayi yu akana patsidwa ndalama yake akana ka otcha nyumbayo kungoti anthu oweluza mrandu aku malawi zimakukanikani imeneyi sinkhani zili ngati ufiti zogonanazi öne mkazi sangango fikila kuti tiye tikanyengane kumuuza mamuna anayambitsaso nkhani yoka vulana ndi bambo khothi lakanika kuzenga mrandu mwinaso mayi yu poti analibe ndalama yokadisa ku khothiko kwaoweluza mutayeni mayi siwolakwa olo kuli n.dalayo akudziwa bwino kuli ieko kuti sanapange bwino apolice akana bwanji kumu ulula pamenepa akudziwa bwino bwino chilungamo zandi nyasa bwanji chifukwa munthu ali ese amadziwa kuti galu ukanponda nchila amakuluma iwe ndiku kanponda dala nde unga mayankhule kuti galuyu ndiwa chiwewe pomwe chiwewe chita choka kwaiwe sibwino pofuna ku gamula mrandu prz ku malawi osama ona kuti aujeni wa poti ana chenjela munthumba ndetika wakumbukile kukhoti ndiza pathako izi ndi ufiti chigololo sapangila pagulu pofikana kuti zitheke sizikhala zamasewela ayi ndi bamboyo olakwa pamenepo nkaziyo ndiwa bwino bwino ma hule samalola amafuna upelekeletu ndalama osana pange chili chose nde mayi wa kunali kutopa olo ndili ine ali ndi mwayi galu ameneyo olo akana mudikila amu otchele ku modzi zobayo apolice so aku malawi ndinu zitsilu kuphatikizaso ndi akhothi mwina kapena chifukwa choti ntchito zama siku ano mumango patsana kuntundu ndimbuli zomwe zoti ku maphuzilo sizinapite uzi ona zili ku police akuti zikugwila ntchito mukungo tipaka manyi simukumatha zokha zokha zama buzi anla

  10. MUNTHU NGATI UYU SIOFUNIKA KUMUSEKELELA ,MAHULE SIANTHU OWAPATSA UFULU , I WONDER WHY THE GOVt HAD DECIDE TO RELISH THESE INHUMAN LADIES . JUST TRUSH ALL THE BITCHES NOW AND WE’LL HVE A BETTER MALAWI.

    1. Ukapanda Mano Usamaswe Phale Ngat Suenda Usiku Kulibwino Kungokhala Phee Azimayiwa Aliso Ndubwino Wawo Ngat M’modz Walakwisa Sionse

    2. AAA KOMA IWE ! KUGONA NDI MAHULE NDIKUMENE KUKUPANGITSASO KUTI MA PROSTITUTES AZIPEZA ZISANGALALO KOMA ZOPANDA VISION .AZIMUNA NGATI INU NDIAMENE MUKUPANGA FACILLITATE PROSTITUTIONISM IN MALAWI .

  11. vuto ndiufulu apasidwawo nde akuugwilitsa ntchito molakwika,muziawuzanso kut munthu akakhala ndi ufulu amakhalanso ndiudindo

  12. Mukumanyenga mahule ndeosamapatsa ndalama et akamakuonchelan manyumbamo nde muzamanga apolice inu ndikhalidwelanu lomanyengela mphavu pasana panu mwanva

  13. Hule,sanalakwe azibambo mumatiyalusa kwambiri chomupatsira map akunyumba hule ndichani???.azibambo amasikuano ndi ACHISIKA.wawachitabwino.

  14. Akuti anagwilzana ma round awiri ndi chingosha, koma game ya chiwiri ili mkati zinasintha, ada aja mkudya maround 4 plain, hule ameneyu amachaja k150 per nyekhu. Mpomwe panayambira nkhani….

    1. K150 per nyekhu, mmene zikunvekera mkuluyu analipira ya ma nyekhu 8, iyeyo ndikumenya ma nyekhu 21. Moti inaontchesa den ndi,defecit ya 13 nyekhu’s…amalawi ena kufuna udolo paliponse uyu waziona.

  15. Akuluwo anapita kukagula malonda koma alibe ndalama? Hahahahaha! Anamuputa apa court lakondera. Mkuluyo anachitayo ndi theft by trick. lol..

  16. Sanavane mitengo mphongo imafuna kusiya ka mpamba kandiwo wana amavuta akafika opanda ka bonya .hule amafuna waleti yose, kkkkk akabwela m’mwana kukaidiko kuli adzongue adadyela kale ma 1000 MK.

Comments are closed.