Maso a amalawi ali tcheru ku bwalo la ndege la Kamuzu

Advertisement
Peter Mutharika Ethiopia

Chichokereni mu nthaka ya dziko la Malawi mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika pamodzi ndi omutsatira pa 16 September chaka chino kupita ku United states of America, Maso a amalawi ali tcheru kufuna kumuonanso atamusowa.

A Mutharika akuyenera kufika kuno kumudzi dziko limene amalitumikira lero lamulungu pa 16 Okotobala malinga ndi chikalata chochokera ku nyumba ya boma.

Peter Mutharika Ethiopia
President Mutharika fika lero.

Kukhalitsa kwa mtsogoleli wa dzikoyu kudadzetsa mpungwepungwe pamene anthu ochuluka amafuna kudziwa za komwe iye ali ndi zomwe akuchita koma amalawi samakhutitsidwa ndi zomwe nduna yofalitsa nkhani a Malison Ndau amanena kuti a Mutharika akugwira ntchito zothandizira kutukula dziko la Malawi pomwe samatsindika za komwe iwo ali.

Anthu miyandamianda akhala ali tcheru maso awo pa khomo la ndege 1 koloko masana kuti awone mtsogoleri wawo yemwe anamusowa kwa nthawi yayitali atapita ku dziko la chilendo.

Kufika kwa a Mutharika, kukhala kokwanira kufufuta kotheratu mphekesera zonse zomwe anthu anali akukamba kuti sakupeza bwino m’thupi ndipo ali ku chipatala, enanso amati a Mutharika ali mwa kayakaya uko kumene anali.

Mtsogoleriyu adachoka kuno ku Malawi mwezi watha kupita ku msonkhano wa atsogoleri a mmaiko osiyanasiyana (United Nations General Assembly) ku America, koma adaonjezera masiku ake okhalira ku dziko la chilendo ngakhale masiku a msonkhano adali atatha kale.

Nawo atolankhani ali tcheru kudikira kuti awone ngati akanizidwe kudzakumana ndi a Mutharika kapena ayi pamene pamamveka kuti kufika kwa a Mutharika kudzakhala kouma ku nkhani ya uthenga pomwe “pakumveka kuti atolankhani sadzaloledwa kufusa mafunso mtsogoleri wa dzikoyu”

Koma a ku nyumba ya boma atsutsa manong’onong’owa, ponena kuti pulezidenti Mutharika ali okonzeka kulankhula ndi atolankhani.

Advertisement

357 Comments

  1. Taona anthu osowedwa ife, ndiwo anthu amene utsogoleri wao udachokeradi kwa mulungu. Osati izi ayi, sichimomodzi opanda president yapa.

  2. Akumapita kukapempha chinthandizo ndiye kumati boma langa muli .njala ndiye ndimafuna ndalama kwapasamo akukamangisa nyumba zawo achokedi loko atamwalira vuto palibe mungadandaule ndi inu osadulidwanu atumbuka opanda nzeru pussy funk your president

  3. Pa chichewa pali mawu omati “mawu msamatha” tsanu onthu wena ongutha mawu koma dala sibwino ntha zina kuti ozanu okutameni. Galimoto imaphweka okamayendetsa wina onthuni.

  4. Kkkkk akapalamula mwayankhulatu si fisi wa satanism uja amamutchukitsa a koma akunama tilinayenaye pa 2019 pa ma vote ake tamusungila azapitilizatso kuwadyetsa atumbuka onse zitete kkkk pantumbo pa tumbuka.

  5. ameneyu kuno sikawo ofunika apatsidwe 30 days muziko lathu lino,dziko la masiye lino atsogoleli amangopanga zomwe iwo akufuna, cz amalawi timapheledwa ufulu olankhula ,President akakhale dziko la eni mwenzi okwana ndithu ,osaopaso anthu amene anamuuika pa ,pampando

  6. Satana nthawi zonse ndiwolephera, welcome Mr president, ife tili nanu, zikumuwawa akachite report ku police yomwe ali nawo pafupi,DPP chipani chawanthu.

  7. Mphindu lake lilipo coz iye ndi tsogoleli wanthu wadziko ndiye ali ndi phindu osawona phindu lake ali ndi vuto coz petter sitindingamufanizire ndi yesu coz yesu ndi mwini moyo munthalika ndi tsogoleli chabe

  8. Osati kumusowa koma afotokoze kwa mtundu wa malawi momveka bwino kuti nchifukwa chani watha nthawi yaitali chotele? Kenako adauza ife ngati amene tidamusankha?ngati ayi nchifukwa chani adapanga mwayenkha?kumbukilani kuti tsogoleri ndi otumikila anthu osati opanga zinthu mwayenkha

  9. Ineyo ndili ku BT airport ndikudikila a bwana. Kaziwanga ndamutumiza ku LL airport Kut naye akagadile kumeneko.panopo sitidikila ma repoter ayi.tizionele tokha.

  10. Akuti atitengelako masola ayi vuto lamagetsi latha sopano ……anyamata mutani makasu m’manja tikayike nyasi zakhalitsa zikununkha kkk

  11. Thats only the news I gonna like, not about humanity but Holy spirit, remember faith comes from hearing the word of christ(Romans 10:17)

  12. nkhumene.amadyelandalama.simakuziwa.mukulimbanazithu.zazzz.kodi.munafusaakubanjakuti.wawoanatisiya.mukuchulukitsa.kutokota.kapena.amapkupatsani.simandiye.pangani.zithuzoti.mupange.ndalama.osati.kutaya.time.ndizinthuzotisim

  13. Mulungu ananena musulat yasini kuti amaika paudindo unthu amene wamufuna panthawi yake ndpomso amatha kuchosa munthawi yomwe wafuna ndiye chomwe tingaziwe inu ndi ine tilibe mbavu zochotsa peter paudindo tiyeni tiyang’ane maso kwamulungu ndipo mavuto a2 azachepa peter ndchabemso pamaso pake,

  14. kodi ndi bwino kumafunila anzanu zoipa?Afe ameneyo,mau amenewa akuchokera mkamwa mwa a Malawi ozitcha opemphela ,oopa mulungu.Nzomvetsa chisoni kumamva ndemamga ngati zimezi kuchokela kwa anthu oopa mulungu koma mphamvu yake adaikana. Ena mwa inu ndi mamembala a machalichi otchuka amene akumanamiza anthu kuti mulemela kapena kuti mavuto anu atha.

  15. Ndi Fumu ya Dziko Yesu Chrisitu bansi, Tonse Ndife Maliro, Kaya Wina Amayenda Ndi Bodigad Mumbuyo Amenewo Phindu Palibe, Ine Kuchoka 2008 Ndinapatsidwa Mtendele Wa Mtima, Koma Ndinaudzidwa Kt Ndisaiwale Malango Khumi Aja, Ife Si tinga Njenjeme Ndi Munthu Obadwa Ndi Munthu Mzake Ai, Kukanaveka Mbili Yoti Kwalira Lupenga Ine Ndikana Njenjemela, Koma Zandalezo Inafe Tinaluza Makolo Anthu Nkhanizake Zomwenzi, Pitani Mukamulandile Mukalowe Naye Kumwamba, Ife Sititama Mukono Wanyama Ai, BRIV TO SPRT, HE HAS MADE YOU

  16. Eni Ake Tinamuvoterafe Tili Phee Ndipo Tizamuvoteranso,inu Mungobwebwetuka, Simunati Mukhaura Anthu Odalira Kupempha Inu Mutambulenge,

  17. nthawi zonse apresident amapita kunja kumisonkhano and sipankhala zoyankhula zambiri and ngati akubwera dziko lonse limatekeseka ndi kubwera kwa tsongoleriyu,,,,and akafika amayenera kulandira ulemu wapadera asanayankhule kenaka anena zomwe watibweretsera kodi lero chikuvuta ndi chiyani,,,,nanga ngati ali moyo sanamvepo kuti anthu akuwaganizira kuti amwalira bwanji osaonetsa ku mtunda wa amalawi mwachangu kuti ali ndi moyo,,,nanga ambali ya boma bwanji mwagoti ziii

  18. zundimvetsa chisoni coz Malawi yenseyu palibe amene akuziwa za apulezident athu. bolaso mpiratu mmatha kulosera kuti atawine ngakuti. kwangosala 45m yokha kuti tiziwe zoona zake…..

  19. Chitsiru chosalabadila anthu onwe anachiyika pa mpando…..Bambo akachoka m’nyumba ndikukakhalitsa komwe anapitako amayetsetsa kudziwitsa banja lake chomwe iye wachedwela……mbuzi ya munthu

  20. Welcome home mr president we luv u, ena kumasangalala kut wamwalira en nw hearing dat he is coming here in sound health so frustrating, long live mr president

  21. Koma bakha ameneyutu akafika afusidwe mafuso ndi atolankhani osati angopitilila kunyumba kwake chifukwa watiwonongela ndalama zambili z.

  22. inuso a 24 ndizisilu.ndiomwe mumayakhura zambiri zoti wafa.munakhala bwanji?zolemba zimakusowani eti?koma afe achakazanu or amu tiwone ngati mungasangalale.ifeyo peter timamunyadira and ndiyemwe amatisogolela or sitili kumalawindikanakonda peter asayakhure ndi mtola nkhani aliyese coz ndinu zisilu zanthu.mukasowa cholemba muzingopita ku toilet

  23. This president if at all z alive,is self centered osamva and extravagant, Last year msonkhano ngati womwewu ananyamula anthu ambiri plus mafumu. He was blamed for that but this time akupanganso zamkutu over spending while we r in problems here.

  24. Malawians want hin dead but God wants him to live so that he can save poor people. .. stupid Tumbuka hyenas want him dead. .. kubadwa mtumbuka ndi tchimo… umakhala onyansa zonse…. atumbuka ndi zinyama zoopsa…. munthu kuwachitila zabwino sayamika… anangokula mitu kma ndi nkhumba zopanda ntchito…. ali busy kunena kti Peter wamwalira …. the only president with vision. .. mukamati athetse njala mutanthauzanji? sakukuzani za ulimi othilira? mukufuna azizakulimilani? ? kodi iye amagwtsa mvula? mukukhala ngti ku USA ananyamula makasu anu…. kapena anatenga chanu chokodzela chanu kti uhule simupanga….. a Tumbuka mbuzi mbuzi… tiyamba kukuphani….. inu a chewa nde kaya sindinena zambri

    1. We’re all malwawians don’t discriminate bcz if u carry on saying that you will make things worse. You telling me that all who were talking about Peter are tumbukas? You bursted

    2. ofcorse ,do think all tumbuka are stupid to u, then if u r better to them wt hv u done ,about ur father mnthalika for going to USA ,just worsing money for nothing ,go to hell with ur fakiiii father

    3. you Raymond Chimbala, last time u commented the same bullshit and today you do the same..but to day i will choose to ignore your primitive tribal “bigotry” comments but u have to note this: we are watching your stinking comments very carefully and wait and see your harvest very soon. mind you, ” still waters run deep” today i’ll not comment much like i did last time. you cruppy and wretched son of evil one!!! next time we will be fed up… .

    4. you chewas fulish ,and you guyz yo busturd chifukwa chake umbuli kuuchewako ukupitililabe coz ndinu anthu osazindikila palibe zomanyozanaapa olo ku sankhana mtundu,oky wary not akanat wafa ndikanadya phwando coz mwapitala mulibe chonde zausogoleli tsakuziziwa.alindi dwela kwa eni.

    5. Ndipo uziwalemekeza aTumbuka coz mawa akakuthamangisani pamene mkufunsira ntchito kwao,yolima fodya.Ife ndife mabwana anu mwaiwala!.

  25. Hello friends, my name is Susan Mwanza this a testimony of how i got cure fully from HIV/AIDS, i was diagnose with HIV/AIDS FIVE year ago, i contacted a doctor who later gave me some treatment, but it was like the treatment he gave to me were not enough i was desperately in need of something that will get rid of the deadly virus from my body, my life was miserable i lost my job and few of my friends, not quit long a faithful friend of mine came to me one afternoon telling about what he saw on net a testimony of how DR Abumen cured people from various kind of virus including Herpes, i was like this is a scam, but he old me he believe in what he had read on line’ he told me he will contact DR Abumen on my behalf and he did so, after some days he receive a parcel containing DR Abumen herbal medication, he present it before me to use it, that when am cured i should pay back the money it cost her while negotiating for the medicine, after taking the medicine for some days according to DR Abumen instruction, then i decided to go for check up and i was happy to see that no sign of the virus was found in my body, i am very thankful to my friend, if you are having a similar problem or you need his help you can reach him on ([email protected]) or you can call or chat with him on whattsapp through +2347085071418, please share to save life.

  26. Kubwela kusabwela ndichmozmoz bas okadikilao alibe zochta apidula chan pussy ameneyo abwele komwe anali olo titakhala opanda pussy yo zkusiyana bwaj amaleka kufela koko bwaj

  27. Apopo nde eeeee kaya komano asabwere ataseka maso we want him to pay back pliz ngat atabwera ataseka maso ndie ndi waku Ndatha farm

    1. nanunso pantundapo anabere inu???mumafuna kuti akhale president wabwino azikukugulirani ndiwo zakunyumba kwanu??hehehehehe nsiyeni nzanu ngati akuba akumaba chifukwa chamaphunziro ake,,,anachita kulimba kuti akhale president

    2. mmmm komaaaaa maphuzilo asakhla kubela,,za miracle kupanda achair analindani onse ndi mkuluwake amalemu 2,asova ndi maphuzilo awowo,,,lero yasla 40 minuyes

    3. #Blessings tiuzenitu mesa ati wafika nde he’s dead?????akakhala malirowo onse omwe akumufunira kuti amwalire akadya malirowo komanso nawonso ziwachitikire kunyumba kwawo muone maliro momwe amaopsela

  28. ovutikafe sitinamusowe ndi chani chimene angatipindulire kwa anthu osauka ngati ife zoyenera anthu a ndalamamanu zimenezo

  29. Inu nonse achingolopiyo ,asaona aku Yerico perekani ulemu kwa nsogoleri wina aliyense wa dziko lino kaya mlomwe. Batumbuka , machawa,mitonga masena .msogolwri wa dziko sachepa chifukwa amakhala ndi mphavu zonse ziti atha kukusaukisisa or kukupasa mavuto mpaka ukakhala kuti ndiwe zofuna kudziwa akulankhula. Koma achingolopiyo yonse sitingakhale ma president ayi chauta amasankha pa nthawi yache.Ngakhale mutanyoza bwanji inu ndi ine kwathu nkulira basi

  30. Ndilibe Naye Ntchito Akagwere Uko Palibe Chosintha Kubwera Kapena Kukhala Konko Mumuuzeso Kut Asabwere Kuno Malo Kulibe Tidagulitsa Akhale Konko Shut Up Sitikumusowa Ayi Tizikhala Mwachonchimu Opanda Iyeyu

  31. Ndinu zitsilu inu a malawi 24 mumalemba nkhani za bodza mkusokoneza anthu mitu lembani nkhani yomwe mulinayo ndi umboni kale ninkaesa mumalemba zowona ndinu zitsilu kwabasi

  32. Sitinamusowe (except ma cadets mwina ndiwo amusowa). All we r looking after is to hear komwe anali, zomwe amapanga & y he went AWOL. Alongosole momveka bwino. Kungoononga ndalama za boma basi mmalo mogulira mankhwala mzipatala.

    1. kungoti anthu ena amafuna kusokoneza maganozo awanthu ena we must know dt everyone has its opinion never mind odrs opinions mind urs

    2. mukudziwa kale abwana apa aliyese akupeleka maganixo ake nde wina amafuna adzikuonetsa iweyo ngati fosha ngati iwe uli ndi comments yako osangolemba bwanji naweso

  33. Hello friends, am Anthony Maqebelo by name, i was one of those millions of people living with HIV, i received my breakthrough with the help of Dr Olumo whom i met through the testimony of someone he has helped, after some series of conversation with the person sharing the testimony i decided to contact Dr Olumo which i did, after some negotiation he sent me the medicine with an instruction on how to use it, i notice some change in my body when using the medicine, after completing the dose as instruct i went for test only to be confirm negative by the doctor after the result came out, words on the internet can not express it all, if you are in the same condition and you are looking for a way out of it you can contact Dr Olumo on his email address, [email protected], or you can call or whatsapp via +2348138956767.

  34. Hahaha abwera wamoyo kapena…..????….Nanga akatinamiza titani?….nthawi yatha kale apa…amauser money yathu nde tikuenera kudziwa chililichonse chokhudza iye…abwere ayankhe mafunsowa…kwa ine nde bola angokhala konko coz palibe chomwe wapanga pa dzaka zapitaz…#

    1. kkkkkk eyetu boss…nde enafe sitimachedwa kulankhula penapake pakalakwika…kkkkk koma za ndalezi ndikumanzere boss.

  35. Kod Ndiye Chikukhuzen Ndichan Or Atabwela Atafa Ndi Mmbale Wanu..Kapen Budjet Yamakomo Mwanumo Amapanga Ndi Iyeyo Nde Sanasiye Ndalama Y Amalawi?

  36. I Miss My Prezdent! Welcm Back Mr Prezdent……. Koma Mbuyo Mwanu Muja Anthu Anka Mudali Mukudwala! Koma Tikudziwa Kut Ankangopeka….. We Love You Mr Prezdent, Muaaaaa!

  37. mwayamba kusintha zichewa mesa padzulo paja mumatiwuza kuti wamwalira lero mukuti amalawi tikudikira kubwera kwake. ndiye tiwuzeni zoona kuti tikudikila munthalika kapena mtembo?

  38. Mmaso mwachambwiyanu ndinu.. mesa mmati wamwalira… simunati mumva mbebe..ife tiri ku Airport konko kuti timulandire…. afisi inu mwagwa nayo amene atafe ndi ambwiyanu.. our president is alive and will rule this nation until 2024 … DPP WOYEEEEEEEE APM WOYEEE

  39. Ine sindikumvetsa za kubwera kwa bwanawa , news ina mukulemba za ku Lilongwe komanso ku Chileka airport ndiye tilowele kuti?

  40. odala ndi anthu amene akuembekekezela kubwela kwa Yesu mkhilisitu munchoonadi,pakuti kubwela kwake nkopindulisa.ndi phindu lanji lomwe Peter wa Mutharika afike nalo lelo kubwalo la ndenge?kodi anthu amene akugona ndi njala ayamba kudya chifukwa choti iyeyu wafika muziko muno?kubwela kwakwe kwa Peter kulibe phindu kuntundu wa Malawi.moo wanga ukuyembekezela kubwela kwa Yesu chifukwa nkopindulisa.

    1. nanga kuli ndi phindu lanji kubwela kwakwa?poti anthu omwe adawasiya osauka ndiosaukabe,ndipo omwe adali olumala ndiolumalabe,koma kubwela kwa Yesu mkhilisitu kudzachosa zowawa zonse.#Mniembilee Ausward WaChelse

    2. Mr Andrew Nuxwe Chirwa ngati ndikunama nenani pomwe ndanamapo,komati mukudziwa kuti sndikunama y mukunyoza?idont hv ur tym mr God bless u.

    3. akulu kubwera kwa bwanawa kuli ndi phindu.phindu loyamba ndi kuchepetsa ndalama za boma zomwe zikupitilila kugwilitsidwa ntchito kunjako…phindu lina ndilokuti abwanawa azapitiliza ku gwira ntchito zao zaboma…ngakhale m bible atsogoleli adziko analimo…achina sauli ndi anzao…do you think zikanachitika chonchi nthawi ija ya china sauli anthu sakanadabwa…muli ndi uthenga wabwino bro koma mwaubwelesa molakwika.. God bless u

    4. my sis harriet yesu sanali ku sankha malo yolakira ndipo mu pemphero ananena kuti ufumu wanu ubwera nichifukwa ciani ananena mau?, maufumu ena analiko panthawi iyo.

    5. Harriet Jere,mau aMulungu akuenela kulalikidwa palipose pakuti ndicho chinthu chofunika kwambili.Yesu ankalalikila ngakhale mahule ndiokhomesa msonkho nde pali kusiyana kwanji?kodi inu mutafa lelo mutha kuiuza infa kuti yabwela nthawi yolakwika?nanga bwanji mukuti ndabwelesa nthawi yolakwikwa mau AMulungu?

    6. Awa nde mau amene andigwira mtima.Amalawi kupusa mmene dzuwa likuotcheramu wina kaliki liki akuti akukalandira mtsogoleri amene anapita kunja kukalandira mankhwala chonsecho wasiya mzipatalamu muli mavuto osayamba.

    7. Mr. Patrick Katsabola. Zikuonetsa kuti inuyo zadziko sizikukhudzani, koma nchifukwa chani mukutsata nkhani zandale? Tsamba mwapanga comment li likukamba zandaletu limeneli. Sikuti amene ali interested ndikubwela kwa a president ndiye kuti chauzimu alibe.

    8. Harriet Jere,ine sindidaweluze munthu koma ndikulankhula chilungamo.chilungamo changa ndi ichi.monga mau akunena pa Luka 6 vs 21 mpaka 23 akuti ndiodala anthu omwe ali osauka chifukwa ufumu wa Mulungu ndiwao,komaso akuti ndiodala omwe akunva njala chifukwa adzakhuta.nde kubwela kwakwe kwa Peter kulibe phindu coz anthu omwe adawasiya akutika awapeza akuvutikabe anjala ndi anjalebe,olumala ndi okumalabe.amasiye ndiamasiyebe.koma Yesu akadzabwela zosezi zidzatha ngati mudamudikilila munchoonadi.

    9. True that Ken…kodi yesu ankawalesa anthu kukhuzika ndi nkhani za boma…mukuweluzatu atsogoleli mukuiwala kuti ambuye yesu amakonda aliyense…atsogoleli tikuwadikilawo yesu amawakondanso nde kukhuzika ndi mmene zilili panopa mmalawi muno si tchimo..instead tionese chikondi kwa onse then it will be easy for a us kulalikila mmalo ngati awa

    10. Mr Ken M’ baya ll u plz tell me y Yesu khilisitu ankalalikila ngakhakhale mahule ndikudya ndiokhomesa msonkho then ill answer ur question

    11. mmangodana ndi Peter yo…that’s why kubwera kwake phindu lake simuliona…comparison ya kubwera kwa Peter ndi Yesu aint right…Pete ndimunthu yesu ndi mwana wamulungu wamoyo it’s obvious kuti yesu kubwera akhungu aona and palibe wanena kuti Peter akabwela olumala ayenda mavuto sikulumala kokha

    12. kuti muone malo omwe mukuchitika za dziko lapasi ambili amakhala nazo attend nde pamemenepo nde pofunikila mau aMungu kuti afikepo.palibe muthu amene amafuna dokotala chosecho sakudwala,odwala ndiomwe amafuna dokotala.komaso y asadayambe misonkhano ya chipani amati tiyambe tapemphela?nanga nchifukwa cha Yesu adasanduza madzi kukhala vinyo chosecho kudali kuukwati osati kutchalitchi?nanga nchifukwa chani Yesu adanena kupita kalalikileni mmiseu mmisika komaso mmabwalo ngakhale mmizinda?

    13. Mawu amulungu alibe nthawi kapena malo, ndcho chifukwa bible limati mwana wa mulungu adzabwera ngat mbava palibe yemwe azadziwe . Odala iye akhala nd njala muuzimu nd chikhumbo cha mawu ake
      .ndatsitsimuka koooowopsa blaza keep it up
      Mulungu akudalitsen
      Za Bingu aaaaa ndngomva kwa Anthu ,
      Za wanga wapamtima Yesu ndilingalira usana nd usiku

    14. what I know is pali mmalemba oyela pamene analembapo kuti kudikilila ntsogoleli wadziko yemwe anthu sakudziwa kuti Ali bwanji ndi tchimo ine Monga mmalawi ndimakonda Yehova yemwe amandiphunzitsa za chikondi ndipo chikondi chimenechi ndimakonda dziko langa that’s why I won’t stop being worried kuti big man abwera what time and Ali bwanji?…that won’t stop me from waiting upon the second coming of our Lord Jesus Christ…

    15. ine sindikuweluza or kukuumiliza or kudana nazo kuti mudikile Peter iwon’t do that,koma iweo usandilese kulalikila mau a Mulungu pakuti ndiofunikila kuposa moo wanga.ukandilesa kulalikila am teling in the name of Jesus christ the only son of God miyala ndiyomwe adzalalikile pakuti chosatheka ndi munthu kwa Mulungu ndichotheka.iwon’t stop to talk more about the second comming of christ its now o never.Ndi Mulungu yekha adzathese mavuto osati mtsogoleli wadziko.Harriet Jere

    16. sikukulesa kulalikila and I like kuti wabwelesa this pa page ngati iyi koma wabwelesa mauwa ngati ukuweluza anthu amene akudikila kufika mziko lino kwa apresident ukuziwa nkutheka out of anthu ameneo alipo anthu opemphela zedi oti their relationship with God ili very fine…komanso mawu amawaziwa

    17. a Katsabola, mu comment yanu muli sarcasm tone yakuti onse amene akukadikirira APM ndiopanda nzeru koma achikhala m’manyumba mwawo kumamudikirira Yesu. Yesu timamudikirira daily koma that does not stop us from engaging ourselves with day to day activities. Inutu mu comment mwanu simunalalikire koma mwaweluza ndikunyoza anthu amene apita kukachingamira mtsogoleri wadziko lino. Inuyo a Patrick Katsabola palibe chilichonse chimene mumapanga koma kudikirira Yesu basi??

    18. Patrick Katsabola, you are very wise person and your post has been of inspiration to me, keep it up telling people about the kingdom of God which is aready at hand…..

    19. hahaha even Jesus Christ new what to say at the right place and right time thats why nkhosa zache sizinali scattered..

    20. hahaha even Jesus Christ new what to say at the right place and right time thats why nkhosa zache sizinali scattered..

    21. Zoti ndi mtembo mukuziwa ndinu what I know is he is God’s creation whose state is currently unknown …kuteleku thats why tikudikila tinve

    22. Akadakufunsani inu funso lija lakuti “kodi nkoloredwa kukhoma msonkho kwa Kaisala kapena nkosaloredwa”…. Inu ndinzeru zake zimenezi mukadayankha kuti “ayi sikoloredwa”, mukadadzetsa chisokonezo ndi mpungwepungwe mdziko. Koma Yesu anali wanzeru kwambiri. Ngati mukutumikira Yesu mudzipemphera akuninkheni nzeru

    23. Inuo mr Ken M’baya ndiomwe mukuweluza pakuti mukunena anzanu kuti ndi achipha maso nanga inuo muli mbali iti?ndakufusani mafuso ambili koma simudayankhe coz u know very well kut am talking the truth n even God knows this.pakuti tonse tinachimwa tilephela kufika kuulemelelo wake.Mulungu akuydziwa ekha amene ali akedi nde musandilese kulalilikila pomwe Mulungu wandiuza kuti lalikila pakuti simukulimbana ndiine koma Mulungu pakuti ine sindiuchita manyazi kukamba zamau ake palipose.komaso ine sindikudzitenga kukhala munthu wangwilo ayi koma kochepa komwe Mulungu wandiuza kuti ndigawane nanu ndikuyenela kukaika poyela.in fact inuo mwandiweluza kuti ndikosaenela kulalikila pa page ino y?kodi nchifukwa chani kunyumba ya malamulo kuja amayamba ndipemphelo?again y ngati presdent wawina amamulumbilisa atanyamula baibulo nkukweza manja ake kumwamba?y amipingo amasonkhana nkumapemphelela kuti dziko lathu lizienda bwino? mundiyankhe

    24. Harriet Jere u wrong n God must 4gv u coz ur mic use the words of God.there is only one God n pa anthu osewa palibe amene wanena kuti iye ndi Mulungu or ine sindidati ndine Mulungu.so what’s the shame like that iweo nkumati sitingakhale Mulungu,iweo umafuna utakhala Mulungu kapena?let God b God.

    25. hahaha zakuwawani atsogo? mawu mukuyesa mmaziwa nokha? kapena mukuyesa olungama ndi nokha…among anthu odikila a presint palinso opemphela and mwati polumbilisa amakweza manja kumwamba presenting them kwa Yehova that’s why this is also the right time to call upon Jehovah alowelelepo pa what’s happening paMalawi pano nt kuweluza anthu odikilila a president tili ndi ntchito atsogo…to interceed for our nation Malawi

    26. hahaha zakuwawani atsogo? mawu mukuyesa mmaziwa nokha? kapena mukuyesa olungama ndi nokha…among anthu odikila a presint palinso opemphela and mwati polumbilisa amakweza manja kumwamba presenting them kwa Yehova that’s why this is also the right time to call upon Jehovah alowelelepo pa what’s happening paMalawi pano nt kuweluza anthu odikilila a president tili ndi ntchito atsogo…to interceed for our nation Malawi

    27. hahaha zakuwawani atsogo? mawu mukuyesa mmaziwa nokha? kapena mukuyesa olungama ndi nokha…among anthu odikila a presint palinso opemphela and mwati polumbilisa amakweza manja kumwamba presenting them kwa Yehova that’s why this is also the right time to call upon Jehovah alowelelepo pa what’s happening paMalawi pano nt kuweluza anthu odikilila a president tili ndi ntchito atsogo…to interceed for our nation Malawi

    28. Harriet Jere nde chalakwikwa ndichani ine kulemba kuti chofunikila kwambili ndikuyembekezela Yesu mkhilisitu?tandiuze iweo kodi utadwala umapemphela kwa peter kuti akuchilise or kwa Mulungu.tandiuze chofunika ndichiti kwa iwe pakati pakuembekezela peter ndikuembekezela Yesu?tsono ngati munymba yamalamulo amayamaba ndipemphelo komaso akawina amamulumbilisa nde ine ndalakwa chani kunena mau aMulungu pa page ino?Mulungu ndiye akudziwa amene alidi ake so don’t tell me kuti alipodi anthu ena omwe ali opemphela munchoona iweo ndi Mulungu kuti uwadziwe opemphela munchoona ndiochimwa?we know nothing about it but what inkow is that palibeso chinthu china chopindulisa pamoo wamunthu wina aliyese pano padziko choposa Kuyembekezela muchoonadi zakubwela kwa Yesu mkhilisitu amene ali mwana wa Mulungu.

    29. Harriet Jere,tandiyankha fuso langa lakuti kodi ukadwala umaitanila padzina lapita or la Yesu mwana Wa Mulungu?nanga kudikila peter ndikudikila kubwela kwa Yesu chofunika ndichiti kwa iwe?utandiyankha plz

    30. eyetu nafenso tikuyembekezela kuza kwachetu atsogo…koma that does not mean kupita ku KIA ndiuchimo nafenso tikuziwa ndi Ana amulungu okhulupilila mwa ambuye wathu Yesu Khristu nde stop acting ngati ndinu olungama pondiweluza… mwanena mwambiri kuti u mis using mawu amulungu I didnt answer that coz I know am nt am just trying kukuunikilani kuti tsiku lina mukamazalalikila pa group ina musazaweluze zaikeni uthenga omangilila osati kuphwasula polalikila mwa chikondi mosasankha mbali coz yesu anawakonda ochimwa amawafikila mosawaweluza ndipo amatembenuka mtima nkulandila chipulumutso…muli ndi uthenga wamphavu bro koma presentation yanu muchosemu ka element ka kuweluza……have a blessed day

    31. stop asking a question with an obvious answer palibe amapemphela kwa Peter nde uzifunsa ukuganiza Peter ndi munthu olengedwa ndimulungu…ndipo reference ya ili poor pokhapo popanga compare Peter ndimulungupo…olo mwana wa 5 years akhoza kuyankha kuti timapemphera kwa mulungu nde musayankhe mwaphuma ganizani bwino bwino komanso afunseni a mzimu oyera akupaseni yankho loyenela musangoyankha kuti muyankhepo basi

    32. nchifukwa chake anthu opemphera we missing the target….spread the gospel and bring people into the kingdom of God…how can that be possible? love from the book of Corinthians .unconditional love tiafikile yes koma nt moaweluza coz tikatelo athawa sabweranso kuzanva uthenga wachipulumutso uja…..

    33. Kodi ndani pa ma komenti osewa wanena mzake kuti ndiochimwa or kuweluza mzake?iweo wandinena ine kuti ndine ochimwa ndipo wandiweluza.iweso ukufunika mzimu oyela kuti akuunikle ndikukuziwisa choona chomwe komenti yanga ikutanthauza.komaso iwant u to know this from now on ukafuna kulemba dzina lakuti Mulungu uziyamba ndi chilembo chachikulu osati chaching’ono.

    34. Palibe kuweruza koma akuphuzitsa ndipo vumbulutso la mlalikiyu nd lakut tisamataye nthawi nd mzadziko pakut ndizothera pansi pano
      Same same bible anthu timalimasurira mosiyana mmalinga nd maganizo nd conditioning yomwe alili sadziwa choona chili mmawuwo
      Bra #Patrick katsabola zikomo pondiunikira choona cha moyo ukudzawu
      Za pta aaaaa sizikundikhudza wandisangalasa ndiwe wandipasa chakudya cha uzimu
      I think you are pastor

    35. Afika a president aja tadziwa ali moyo kwa tonse amene timadikilila nkhani ndiimeneyo…tisaleme kupemphelela Dziko lathu la Malawi…zikomo

    36. Hahaha Mr. Katsabola seems to have the biggest problem, he looks at everything in this life negatively as if there’s nothing good. Ur not yet in heaven Pastor Katsabola, ur still here on earth and by the way ur not the only 1 who believes and awaiting God’s kingdom. Stop ur funny hypocrisy and blasphemy here. Inuyo mukamafika pakhomo kuchokera kotumikira, ana anu sakuthamangirani / kukuchingamirani musanalowe mnyumba “eyaa adad eyaa adad!” akatero ndiye kuti ngochimwa sakudikira Yesu?? Hahaha some people are obsessed with negativity and they are blind to positive life. Case of hypocrisy of highest order!!!

    37. Ken M’baya sumukudziwa tanthauzo lakomenti yanga ndipo simungavesese or pang’ono,koma ndikuyamika Mulungu kuti pakomenti yanga sindidazitche olungama koma ndati ndiodala omwe akuyembekezela Yesu munchoonadi.kodi chinakunyasani ndichani pakomenti yanga?inuo musathe mau or kudzivuta ndikunyoza ine sindidakunyozeni koma inuo mwandinyoza kuti ndine wachipha maso komaso ndili ndi ziwanda, in fact mwati ndine wakhukhu.here is the words if want or not in my lyf chinthu chomwe chili chofunika kuposa moo wanga ndicho kuopa Mulungu,or mutandinyoza momwe mumadziwila koma ine ndili nga pa Yesu no kusuntha.ndipo sindidati ndine olungama ayi koma inuo zaonekelatu kuti mwangodana nane chabe.ineo sindingaleke kupanga post komenti yokhudza mau aMulungu pomwe ndikuona kuti ndingathe.meaning ya koment yanga ndiyakuti anthu asamataye nthawi ndzaziko lapasi koma azikumbukila kuti pali wina amene ali ofunika kuposa amene akubwela ponpano.osati zomwe inuo mukulankhulazo.

    38. Inu aKatsabola simudzamupeza munthu amene satenga gawo pamoyo wadziko lapansi. Munthu ndithupi ndimzimu. By the way ndaona mwamudzudzula Harriet Jere zakalembedwe ka dzina la Mulungu. That was also not necessary coz Mulungu sadzaweluza munthu kuti umalemba motani dzina lake. The most important are those ten commandments. Tidzakapulumuka mwachisomo osati chifukwa cha ungwiro Mr. Katsabola

    39. muli ndi milandu inu inu mr Ken M’baya but its ok choice is yours n me ihv my choice also,so plz musandilese kukamba za kubwela kwake kwa Yesu coz ine sindidakuleseni kukalandila peter.ndipo musandiweluze chifukwa ine sindidaweluze.musandinyoze poti ine sindidanyoze.litchulidwa ndi tiana takuyamba kulankhula nanga ine nchitilenji mantha kutchula zadzina lake.

    40. Mr. Patrick Katsabola mukadakhala ndi mphamvu yoletsa anthu kupita ku KIA lero mukadawaletsa koma poti mphamvuyo mulibe nchifukwa chake mwangowanyoza kuti alibe nzeru popita kukadikirira APM m’malo momadikirira Yesu. Inu mukuganiza kuti onse anapita kumeneko alibe chauzimu? Ena anapita kumeneko kukagwira ntchito monga atolankhani, asilikali, ena anapeza mwai okagulitsa malonda, ena anapitila transportation business, ena anapitila kungosangalatsidwa. Onsewo inuyo a Patrick Katsabola mwawapanga disqualify pa moyo wauzimu?

    41. Mau a Mulungu powagwilitsa ntchito pakufunika mzeru zakuya zedi mwa Uzimu, chifukwa Generation ino ndiya nzeru kale zochuluka so to convince pakufunika kuyankhula modzichepetsa

    42. zoonadi Mac and anzimu oyera ndi a dongosolo pozeka iwo pamakhala bata nde we should ask the holy spirit atiphunzitse how to present mau amene ndi vumbulutso rather than speaking it in our own way…

    43. inu musandiweluze coz ine sindidaweluze,musadzivute muntima mwanu chifukwa ine ndalankhula chilungamo.ndipo sindikuona cholakwikwa pakomenti yanga coz sindidanyoze Mulungu koma inu mwadana nazo poti ine ndalalika.odwala ndiomwe amafuna dokotala osati anthu omwe ali bwino.kamba kamaonekedwe anga simungagwilise ntchito uthenga wanga koma mutha kugwilisa ntchito uthenga wa anthu amene ali olemekezeka ndioyenda ndi bodigadi.tisaiwale kuti Mulungu amagwilisa ntchito munthu amene wafuna komaso nthawi yomwe iye wafuna even pamalo pamene iye wafuna.Mulungu emweo amatenga zinthu zopanda pake kuti zikachititse manyazi zinthu zanzelu.musandidelele kamba kamaonekedwe simukudziwa cholinga cha Mulungu pamoo wanga.mau aMulungu akuyenela kulalikidwa ndiwina aliyese posatengela maonekedwe chuma or umphawi.ndikukuuzaniso kuti pali wina ofunikila koposa amene dzikoli likumuyembekezela amene adzathese mavuto awanthu.

    44. in my comment ididn’t say anthu apita ku KIA ndiopanda nzelu,inuo ndiomwe mwatelo ndipakamwa panu chifukwa choti simudanvesese cholinga cha comment yanga.vuto lili ndi amalawi ndilakuti timakhululupila zokhazo zomwe athu ochita bwino angalalikile or zikhale zabwino or zoipa.koma ine sindidanyoze ndipo ndalankhula choonadi kuti sikuti poti peter wabwela mudziko muno nde kuti mavuto akutha ayi.kuti mupite kumizi even mmatauni anthu akuvutikabe sadasiye kuvutika kamba kakuti iye wafika.nde ndindani amene angakhutise anthu anjala ndikumwesa madzi anthu aludzi?ndi Yesu yekha angathe kutelo,so that is y ndikuti tisamataye nthawi ndizinthu zosala zadzikoli pakuti pali wina amene akudzifunila ulemelelo Kumwamba.Mr Ken M’baya mudapita ku xool in fact mumganiza komasoi mumaona,so ll u plz tell ngati ndikunama kuti Yesu ndiye adzathese mavuto adziko lapasi.

    45. Mr. Katsabola. I never meant to offend u. I don’t hurt other person’s feelings deliberately. I was just trying to present my argument. Take out that inferiority feeling from within urself, I didn’t even check ur profile to see who u are. I could have still presented the same argument even if it were some other famous preacher. It was a pleasure interacting with u Mr. Katsabola

    46. taphunzirapo zambiri pa comment yanu bro…osalema kulalikila uthenga big up…take everything discussed positively and Improve mmwina takonzanamo..ifenso tatelo atsogo have a blessed day….osalema kuyembekezela yehova…Isaiah 40 vs 31

  41. Ali tchelu koma osati loona malilo loona wa moyo osati wakufa nde mudzadzi tukwanitsa bola musakhale mwaika kwa merika konko ndiku panga prastick sajaly ndiku muveka waku banja la amuthalika ndendende osasiyana pali pose ndi piter chifukwa amerika ndiku idziwa bho bho e to z kukhani ya ma sajaly wa sianango gula manda kwa merika ma dokotala amene amapanga za masck yofanana ndi piter amaliza loweluka ndinkani mwapanga kuti afike kuno lamulungu your welcom fake piter muthalika on sunday

    1. Lelo ndi la mulungu gays osama comenta zoti ena aku oneleni ali ese imakhala yolakwa lakwa W umamu ona ngati Z timayaka komabe muku dziwa chomwe ndina tatha uza koma poti nose apa ndinu okula ntima ndinkani mwabwela ndima waizi tieni tidikile a piter muthalika a feg wo basi chifukwa boma lima bisa malilo mukumbukila ifa ya bingu wamwa lila ankakana kuti sanafe komano panalibe njila iliyose yotiphimbila nmaso chifukwa chipatala chake chinali cha sento chomwechi nde awa atipangila pran sinanga akudziwa bwino ango gula manda kwa merika khulupililani akubwelayo si piter ango panga chi prastic sajaly chofanana ndi piter amerika siyama sewela zidza ululika nthawi ina yake mudzamva ndinkani amalengeza zoti amene adzinena kuti piter wafa adzimangidwa aku dziwa ndichimene awumbacho pano n.tsogoleli wathu ndi FANO osati piter koma chidzi endela dzina lomwelo

  42. osati kumusowa koma kufuna kuziwa zoona pazambiri zomwe zikumveka…chinaso ndalama zamalawi zapindula chani.ndiochepa omwe amusowa koma zoona zake zikhala zikuziwika pakubwela kwawo bwanawo.tasala ndi 1hr n some munis.

    1. kkkkkk koma bro remember kukumveka kuti no media nde sitiziwa kuti zili bwanji kumeneko….komaso USA ndisuper power imapanga zinthu zosayembekezeleka.koma we still counting down sunday.1.5hr remains.

    2. nafeso pano tayamba kulizolowela moti kuzalimva kachiwili no problem……ine ndasala ndi 40mns plz kufuna kumva kuti bwana afika uko kumalawi??poti tili kudziko la eni tizimvela mumasocial net momuno.

    3. #Tambala ndemwatukwana muli ndichisangalalotu.ife timafuna kuti abwele nde azisogolela komaso kuuza mtundu wamalawi zomwe wanyamula kwatym yayitali kumene anali.

Comments are closed.