Patience Namadingo trolls ESCOM in Facebook video clip

Advertisement
Patience-Namadingo.

Gospel musician Patience Namadingo has fired warning shots at Electricity Supply Corporation of Malawi (ESCOM) over persistent blackouts.

In a video clip that was posted on his personal Facebook account on Monday, the singer insinuate consequences that may befall ESCOM staff should the situation remain static.

Patience-Namadingo.
Patience-Namadingo. trolls ESCOM.

He hopefully concludes a day is coming when consumers shall know the one responsible for hitting the switch-off button.

“Akazangomuziwa dzina amene amazimitsa magetsi, kungomuziwa nkhope kuzavuta, kungomuziwa yemwe amadina, yemwe amadina, yemwe amadina batani lozimitsira magetsi, kudzavuta (when people will find out the identity of a person responsible for switching off electricity, there will be trouble),” sings Namadingo

The end part of the clip exposes real feelings from the artist as he addresses the situation. He violently plucks the guitar then exclaims, Ndakwiya kwambiri ndi zamagetsizi!

The video is currently enjoying downloads with many people sharing through social media platforms. Feedback has been overwhelming as evidenced by large numbers of people applauding Namadingo for his creative mind.

Malawi is currently experiencing never ending blackouts due to drop in water levels in Lake Malawi. The situation has gone from bad to worse with some areas going for more than 18 hours without power. This has had ugly effects in a number of areas.

Advertisement

129 Comments

  1. Will tht make any difference??….anthu anayakhula kut asagulise malawi savings bank,alipo anamva,there’s plenty example of kusalabada in our govt

  2. namandingo is also amalawian who z facing same problem of blackouts ndiye wangoyenera kuchitapo kathu kosatengera kuti iyeyo he z gospel artist ndi munthuso naye oti achitepo kanthu iweo #hastings #singini ukamufusa namandingo bwaj za climate change ngt akuphuxira ku luanar kwakoko usadxive mzeru kuliso anthu ophunzira kwambiri kuposa iweo nyani galu wachabechabe

  3. zavuta kumalawi tangoganizani fridge zenizenizi anthu ayamba kusungiramo zovala ena kumasungiramo makope amafana akachoka ku xul eeeeee malawi ndima bad news.

  4. In my poor understanding a man of God has a huge role in the society as well. So to me Patience singing this song is no crime at all. Don’t be holier than He guys. Atumiki a Mulungu ndiye ofunika kulankhula pa zinthu ngati izi. If I may ask ndi Umbuli wangawu did Jesus not send His disciple to fetch for a peny to pay tax? Was that not part of social responsibility?

  5. Soka Limakhala Kwa Amene Amaziwa Chinthu Koma Sachipanga,,amaziwa Kuti Ichi Ndi Choyipa Koma Zazuzula,, Apapa Namadingo Wachita Bwino Chifukwa Iyeyo Ngati Munthu Wa Mulungu Aziwa Kuti Escom Yikuzunza Anthu Kulibwino Ndiyizuzulee Ngakhale Ndikampani Koma Yimve Ndithu,, P.Namadingo Wachitabwino Kwambiri.

  6. Malawi needs reform i wish… we should hv a crank-down of all old leaders who previously served a 10yrs term no matter to which political party governing @ that time should exit the open door for youngsters- 4 this modern world needs modern leaders not iron age leadership it doesn’t balance the generations need.

  7. I don’t see why some of u r too emotional .. I think he was trying to entertain us and here u go calling him all sorts of names I don’t know about u but I think the human brain functions in different ways and your brain’s functioning is jus pathetic .. Aliyense akumakhala wa satanic kwa amalawi ambiri .. Who r u to judge tamakulani anthu … Ndipo its true if some of u knew adina kuti magetsi athimeyo munakamupha kumene why do u have unknown hate for nothing .. Votsek

    1. People are fond of making names out of nothing. To me the clip has nothing wrong. Honest speaking what he’s done had to be by all Malawians. Kwathu kuno zinthu sizikuyenda. Both Escom & Water Board akutionjeza kwambiri. On the hand the guy has just proved how rich he is with talent. Zamunyasa ndi zake zimenezo. Palibe akachite sacrifice nyumba ya kwao kuti magetsi asayake. Big up Patience

  8. kodi anthunu munakhala bwanji?uyunso wasanduka wa satanic?kodi mumadziwa bwanji inunso mumakhala konko ku satanic ko?chifukwa amene amdziwa mfiti nayenso amakhala kuti ndimfiti amatambira limodzi

  9. Namadingo know nothing about Climate Change….you have just destroyed your reputation as the gospel artist……shame on you…..ESCOM imagwesa Mvula?….Umbuli wanuwo khalani nawo choncho…..ndakwiya naweee

    1. Naweso nd umbuli wakowo ndno bwanj ESCOM imango onjezelbe electricity consumers yet magets nd ochepa wy!!!!! Iwes usandkwiise ok.

  10. Escom si company yopikisana nayo wanyika ase kkk malo mogwada mkupephera kwachauta apa ukukaimba nyimbo yoweruza wat 4 kapenatu ndinu a illuminati masiku omalizadi

  11. Electricity Supply Commission of Malawi amatero ku zionetsa kuchenjera mwapala nazo apa kkkkkkkkkkk lol abbreviation inavuta apa kkkk

  12. Keep it up old friend that’s the sign of patriotism. Your true son of Malawi. Since you spoke these for the first time in Lilongwe being in electricity for 24 hour. Am blessed, we need such brave and courageous people like Namadingo not always Yes Bwana. We are tied

  13. Ndye magesi angasiye kuzima bcz of mr bombocrat kaya mumamuti nadingo zazi m’malo mot uzikamwa magaz kumidima kwanuko iya

    1. Ngat mulimadolo panganipo kanthu ndipeze mavuto chabwino pakut panu agalu inu chonsecho mumagona mu nyumba zopanda magesi ndye mungandiuze chan inu

  14. Sorry we hv changed the name from ESCOM to BOSCOM(Black Out Supply Cooperation Of Malawi) if we change the name again, we will xplain to the public….soon after America

  15. my dad once sent me to pay electricity bill and i used the money to play airtel car competition. When i got home i explain what i did with the to my dad hoping he will understand but he beaten me. Next day when we woke up my dad opened the door and there was a brandnew car standing outside.We were so excited and in tears. Until we realised that is the electricians with their tools to cut our electricity off. and my dad beat the crap out of me eish #zovutazedi

    1. Muli ndi umboni onse kut ndiwasatanic, naphapo ndani modz mwa inu kwanuko , ok abwana tamva, zomwe mwanenazi , komaso saletsana ai . Nde sibwino kumaipitsana mbiri zonyasa pa gulu la anthu, pamawa mzalakwa nazo

  16. Next time my fellow brothers don’t let things go to point where it can’t be solved #organizeabigmuch n shut down Malawi in so doing thy will respond so quick plz all workers starting from the government labour n thevself employed pipo plz do it n u will blv me thy will take attention on that do it for 3 days no one must go plz plz i beg

    1. hhahaha wrong interpretation of things. So, man of God has to remain quite mkumaonerera zinthu zikulakwika? Malawi sadzathekadi

    2. don’t bac ur self mr #chavula he is a concerned citisen too he has the right to criticise where ever things r not ryt so u expect that a gospel artist must just concentrate on Gospel music wherby he sees that his fellow Malawians r in limbo I guess a big No to #Teamblackouts

    3. TIKANAKHALA KUT TONSE NDIWOYELA MTIMA YESU SAKANABWERA AND MUNTHU WA MULUNGU AMADZUDZULA CHOLAKWIKA AKHUNGU OKHAOKHA SANGALONDOLERANE NJIRA NDIYE NGAT ANTHU A MULUNGU AKHALA CHETE ANGAYANKHULE NDAN POKHALASO MFULU WA DZIKO MAVUTOWA AKUKUMANA NAWO

  17. He is min! Escom is a victim of climate and political change! Until you and me including the Namadingo realize that we have a role to play. (i.e on next polling day or our behavior: environmental management)

    1. What if the environment still stand the way it is now, should we still tolerate this? Think big mr Phiri, Escom has to go for other power generating alternatives we f….cd tired of ………

Comments are closed.