A Mutharika akubwera la Mulungu

Advertisement
Peter Mutharika

Mtsogoleri wa dziko lino a Peter Mutharika amene anakomedwa mu dziko la Amereka alengeza tsopano kuti afika kuno ku Malawi lamulungu masana.

Malingana ndi chikalata cha kunyumba ya boma, a Mutharika amene anapita ku dziko la Amereka sabata zitatu zapitazo akhala akubwelela ndipo adzafika mu dziko lino masana nthawi ikazakwana 1 koloko.

Peter Mutharika
Peter Mutharika akubwera sabata lino.

“President Mutharika akhala akufika amu dziko lino atakhala nao pa msonkhano wa mayiko onse, wa United Nations, komanso atagwila nawo ntchito zina za boma,” atero a ku nyumba yaboma.

Kuyambila sabata latha, nkhani zinatchuka zoti mtsogoleri wa dziko linoyi wagwidwa ndi matenda ku dziko la Amereka ndipo ali ku chipatala komwe ali mwa kayakaya.

Koma a kunyumba ya boma anatsutsa izi ndipo ananena kuti Mutharika adakali wangwiro ndi wamphamvu.

A boma anachenjeza kuti aliyense onena kuti a Mutharika ali pang’ono kufa anjatidwa ndipo akagwila ukaidi. Izi zinapangitsa mangong’onong’o onena kuti mtsogoleriyu sakupeza bwino kupita patali ndipo ena anonjeza kunena kuti a Mutharika basi apitilila.

Advertisement

542 Comments

  1. Dziko la Malawi silizatukuka njilu ndi kaduka ndi zomwe zakula lelo mukuti a Muthalika akubwela eeee pamalawi choti muziwe akhala ndimoyo wawutali komanso 2019 azawina ndithu

  2. Dziko la Malawi silizatukuka njilu ndi kaduka ndi zomwe zakula lelo mukuti a Muthalika akubwela eeee pamalawi choti muziwe akhala ndimoyo wawutali komanso 2019 azawina ndithu

  3. Why must l feel sorry, he told us kudya ziwara ndi mbewa! This the first & last President heard telling people shit speech!

  4. Its a shameful to hear that our beloved president is dead guys tisamangoluza atsogoleri anthu remember Bingu his brother was also past away so let us stop quallering and pray so that satan should stray away from our president……

  5. Vary thankx god tsogolo lamunthu lili mmanja mwa mulungu osati munthu.ambuye ndinu amene muda pulumusa loti mu sodomu ngakhale mudali chipwi likiti.kuweluza ndi kubwezela ndi kwanu.ufumu mumasankha ndinu,ziwanda zonse mumazi lamulila ndinu chosani zoipa pa nsogoleliyu kuti onse omufunila zoyipa muthane nawo.

  6. Gyz znazi tamazisiyen ngat munthu mwatopa naye mungodkla masiku ake amalize osat mpaka muzikafunila atafa mmmmm sambiii…. Muzive nokha mumtima mwanumo kut ndnu ote… Kwinako muptlze nokha.

  7. Gyz znazi tamazisiyen ngat munthu mwatopa naye mungodkla masiku ake amalize osat mpaka muzikafunila atafa mmmmm sambiii…. Muzive nokha mumtima mwanumo kut ndnu ote… Kwinako muptlze nokha.

  8. Akwabwera Bwanawo bola alongosole tsatanetsatane wa zomwe atibweresera kuchekera ku America ngati akanike kutero akatenge khasu akakumbe chitsa.

  9. am born 1994, koma chiyambileni ine kuzindikila palibe ndi mobzi emwe ndi namuva akuyamikila zachipani chimwe chikulamulila thawi imeneyo koma chikachoka ama bola kubwela winaamati bola wachoka uja which miz tilibe kuyamikila koma kunyoza,ndichifukwa chani tinasakha kulamulila bakili kamudzu ndiopa kuchoka kwabakili ndioipa bingu chifunilo chamulungu komaso timati achoke amayi ndioyipa uyuso oipa wabwino ali kuti?tikufuna titenge zanyumba mwaneba akudya dairy nyama ife bwanji sitikudya koma sikuziwa momwe apezela nyamayo tatiyeni tizigwilisa tchito zelu tisakhala after money tisakuziwa komwe zichoka

  10. ambuye muziti khulukila ife athu anu oyakhula mosaganiza kuti inu mulipo uyu nditsogoleli wazochepa koma inu ndi wazonse izi zapasi ndi kumwamba.tikupephani mupase moyo wautali azafe chifukwa cha inu osati muthu olengedwa kwa inu ayi,chifukwa palibe yemwa angazalamulile zikoli popanda zowawa,kodi obwelayo azapanga ndalama zake?tiyeni amalawi tigwade pasi ndikumupepha mulungu ndiye mwini zonse or iyeso akudalila mulungu ndizoona kuti ife athu tidalile iye muthu modzi?chonde amalawi tisachimwe nazo izi

  11. Mmmm! Astanly Mzuwala! Takumvanu Mawu Anu.Koma Lindani Madzi Apite Ndipo Muziti Ndadala.Zonse Zioneka Sunday Akabwera,koma Ndikuona Kuti Mwafulumira Kutukwana Mukanadikira Abwere Kaye.

  12. manyi anu a24 mumatitenga ngat ife siathu.mumalemba khani musana fufuze agwape inu.tikati tizikumana mmakwalalamu miyala bwezi mukuiwona coz mumalemba zonama ndizo panda mayakho.

  13. Abale pompa mwanena kuti mukuthokoza mulungu kuti mtsogoleri wadziko lathu akubwela ndi moyo kumapetoko ndikudzasokonezanso mukuti thank u jesus ife timve ziti gwilani chimodzi god is god palibenso ali patsogolo pake zikomo mulungu chifukwa chowasunga apita ndi moyo chikakhala chilango mudzalanga nokha

  14. The president was found with brain tumor, of which surgery was the very effective treatment, so the H.E survived the brain surgery but he has given 3 months bed rest of which he opted to take that bed rest @ home, for this material moment Saulosi Chilima Veep will be acting on the behalf of H.E, peter mutharika needs our intercesory prayers, since brain tumor survival rate for males is 31.7% it is grace of God for him to survive the surgery.

  15. amafuna kut akayikitse mano mkamwa mwake oooooo mkamwa ma president nanga pachipululu kkkkkk ukabwela sundy adzafa mondy chifukwa cha bp

  16. Koma guys mukuti peter ali moyo mupusa nazo mulira sundayli muwone news paper yazimbabwe ya pa 10 oct 2016 bwanji sanayakhule ekha zasundayzo ngat ali moyo

  17. Chipatala cha mission ku United States of America nkatikati mwa New Jersey chotchedwa Robert Wood Johnson University Hospital kaya chatani

  18. Wina nde kumati nyonyonyo ati mgeme tikumangani mwayesa nthawi ya asamunda eti.kumati mutimanga chifukwa choti tanena kt peter is dead come and arrest me ozandimanga akhale ndan wapolice wake uti moti mavutowa sakuwaona moti azikasaka ndalama zoti alipilire ma registrations a msce nde simunati tipangaxo mademo mwakweza kwambiri maneb mwatijaila sopano

  19. Amalawi mudzafa osauka is just becoz of simuzindikira kanthu, mwina tingofunsa kodi chiloweleni wapanga chani chimene mwaona kuti dziko lasintha, sii Njala kuthimathima kwamagetsi kukweza kwa ma passport ndi kugwa kwa kwacha, mukuona ngati 5 years coming kudzakhara zotani, mudzivutika ndinu amene mumakonda inu becoz u dont know nothing broo, ur full of sheet forsake including DPP president i dont mind munthu osaganiza wantundu wanji zoti anthu akuvutika chifukwa chawutsogoleri wawo?

  20. Whether he comes alive or dead what difference will it make for the millions of poor Malawians people??? Dziko lankhala mphonje abale zachisoni for our country it’s worse than ever. It’s frustrating really!!!!!

  21. Dziko ndichoncho,zonse ndithawi mmene amuthalika amabadwa yehova amaziwa kale.musiyeni mulungu akhale mulungu.muchedwa nazo mmalo mogwira ntchito.

  22. A MALAWI 24 APA NDIYE NDAKHULUPILILA KUT NDINUDI MA AGENT AKUMIDIMA ZIWANDA ZALIRA TSOPANO OZIKUMBIRA DZENJE AZAGWERAMO EKHA MAGANIZO A MUNTHU SI AKUMWAMBA UA ASHMED KAYA AKUKUTUMAN KOMA MANYAZ MUKHALE NAWO NDI BEZEBULUYO UFUNILA BWANJ IMFA MTSOGOLERI WADZKO YO PLANS AR NOT GOING TO PASS IN JESUS NAME

  23. Manyazi bwanji? The devil is a liar Mutharika is here for 5 years whether you like it or not. I will be there to welcome him

  24. Hello friends my name is Mathew Maketho I was one of those millions of people around the world suffering from HIV/AIDS and and i was healed through the help of DR Abumen I was diagnosed with HIV/AIDS in 2010, I had no hope and felt useless. All these negative feelings quickly suppressed my body immune system and my body started to deteriorate quickly with physical signs of rapid weight loss, my story began to change for good when i met DR Abumen through a woman’s testimony, he sent me an herbal medicine which i took for some days, after taking the medicine according to doctor’s instruction I went to the hospital to get my blood tested for HIV/AIDS. The doctors were amazed when my first blood test result came back negative. They asked me to go back again for another test, which I did and the result came back negative. The doctors could not believe still,To cut the story short, “DR ABUMEN HERBAL MEDICINE HEALED ME COMPLETELY WITHOUT A TRACE OF THE DEADLY HIV/AIDS VIRUS IN MY BLOOD” am so happy, am sharing this to the world to save some lives, believe me there is a cure, you can contact DR Abumen on his email address [email protected] and you can also call or whatsapp his number which is via +2347085071418.

  25. mukati anakomedwako mukutanthauza chan makape inu peter munthalika apart from kukhala presdnt wa dziko lino muziziwa kut wayenda maiko okut inuyo olo mutawagulisa amayi anu kwa anthu asatanic tindalamato sitingakwane kuyenda momwe peter wamunthalika wakhala akuyendamo umo komanso musaiwale kut mkuluyu alinso ndi nyumba zake ku amelica pamene inu olo kachiduswa ka malo mulibe makape ana odyesedwanu nthawi zonse mumapanga phokoso ngat mumaziwa mtengo ogulira tomato bwanj nkhan ndiyakut ndinu amphawi kapena tinene kut mulibe kanthu thts y mukumapeka nkhan zabodza sinanga mulibe chochita chen chen zitsiru pakut panu mwamva haha welcome back my presdnt wow

    1. The story iz that he iz President of Malawi & he must look after his people NDE iwe ukukamba zachuma chake bwanj ? Don’t be weak in mind by mixing stories

    2. @ #Kamwendo iwe ndichikape et tawelerenga bho bho mesa akumudisa president kut anakomedwako ku america ndye langa ndifunso kod president yu ndkoyamba kupita ku america? Musaiwalenso kut ku america ndkomwe iye xul yake wakhara akuphunzira konko ndye mukut anakomedwako mukuona ngat amagona ndi njala ngat makape enanu

    3. Aaa BOMBOO iwe kunyadila ukanyadile peter muthalika, ma milion angat aboma omwe waononga pa chiulendo chachitalich mdziko mwake muli njala? Osamalankhula kufuna potchukila ndeukape umene, p mthalika is the first faken bushit prasdent in malaw.

    4. Aaa BOMBOO iwe kunyadila ukanyadile peter muthalika, ma milion angat aboma omwe waononga pa chiulendo chachitalich mdziko mwake muli njala? Osamalankhula kufuna potchukila ndeukape umene, p mthalika is the first faken bushit prasdent in malaw.

    5. Aaa BOMBOO iwe kunyadila ukanyadile peter muthalika, ma milion angat aboma omwe waononga pa chiulendo chachitalich mdziko mwake muli njala? Osamalankhula kufuna potchukila ndeukape umene, p mthalika is the first faken bushit prasdent in malaw.

    6. Aaa BOMBOO iwe kunyadila ukanyadile peter muthalika, ma milion angat aboma omwe waononga pa chiulendo chachitalich mdziko mwake muli njala? Osamalankhula kufuna potchukila ndeukape umene, p mthalika is the first faken bushit prasdent in malaw.

    7. Hahahah ngat mukut ndkape ndye anawina bwanj or tingoti ku malawi konse kulimakape okha okha et nanga zngatheke dolo kumuika kapena pa mpando onona ngat umeneu Hahahah i love my presdnt Peter inuyo wanu ndan Hahahah

    8. Ma men the one you called your president is a bullshit and you as well…..we have got frequently blackout here yet he spent our tax money in useless journey like that.

    9. Kod?.Umakhala kut aise kuno mages samazimatu Oooo kapena ndiwe mfana wamugetto et mkona akumakuzimisiran makape inu ife kuno mages anangozima mu december last year but thz year sanazime musanamizire boma man plus kuyambila lero ngatidi uli mamuna usamadalire boma kut lizakupezera chochita ngat kwanuko muli osauka bas muzafa osauka uludandaula za forex nkhan yowononga forex yayamba lero? Olo utakhala iwe presdnt ndalama ungazisekerere mxie galu

    10. Mages ndkumangomva kut akumazima kod?.Ndye kut ndzoonadi et ndye tandiuzen akumathimisa magesio ndi Peter or Escom cz sndinamvepo kut presdnt amagwilanso ntchto ku Escom nanunso kunyero kwanu mwamva ana amphawi inu kuzolowera kupemphesa mumativutisa kutipempha tikakwela magalimoto anthu agalu inu mkona akumakuzimisiran

    11. Amwene kupita mayiko ainiwake zopanda ntchito/ koma pitala mathanyulayo akugwilitsa ntchito ndalama zathu za msonkho kumapita kunjako! Zitsilu ngati iwe zosagwila ntchito zimalankhula kwambili komanso president wantundu wanji otisiya ife mavuto iyeyo nkumakasangalala Kunja?

    12. Hahahah anthu osauka nthaw zonse amalimbana ndi presdnt koma anthu andalamafe or presdnt apange zopoila ife sitidanda cz zanthu zinazaza kale m’ma bankmu

    13. So it seems u gat money stainly 8! We all lv our president,but we r talkn abt leadershp…ofcz the president alibe tym yokagwira switch,bt u need to thnk,kukhara ndi ndalama ku bank kwanu it doesnt matter…..we alk hv money koma sikut mpaka ena avutike,khalani ndi umunthu baba

    14. Umunthu ulipo man sndmasowa kanthutu ine ngat mukut mages akuvuta Eetu kaguleni ma generator mtaun mu alimbwe akudikira inuyo

  26. muzitukwana a news day kuzimbabwe osati amalawife chifukwa mmalawi ndiwodandaula chifukwa olo abwele kaya wamwalila tilibenazo tchito chifukwa chikhalileni pampanduwu palibe chanzelu chomwe chikusitha ndiye palibe chotitizikodwelela apa

  27. mwachita manyazi!! mmayesa ngati mutenga udindo,DPP ndi boma mpaka kalekale! a malawi24, ndinu oipa ofunira mzanu zoipa.mulungu akuoneni,ndipo akukhululukireni

  28. When people don’t know what’s good on in life they speculate…. when think they know. .. they fabricate…..and when they do know they hate themselves for knowing the truth. As of now the Peter is the one sitting on the throne. Haters may you please take a break.

  29. Yeeeeeeeeeeh wamubible ndi ameneyo muneneli waukaso kwakufa Peter de great man palibeso khalani ndi timapulofeti tanu tabozato

  30. Tili osangalala akabwela ndi moyo omwe mukufunila zanu ifa inu siosala pa ziko pano mukudikilaso ulendo omwewo mukufunila zanuwo tiyeni tingochivomeleza kuti masiku omaliza chilichose chizakhala chovuta tisade president kuti sakukoza zithu mpaka kufunila ifa nanga akafa omwe angazalamulilewo azalalmulila phavu ya mulungu kapena yasatana? Chenjelani ndi agalu olusa khalani oyela maso muzaziona bola tose mulungu atisunge ndi moyo

  31. A malawi 24 zakunyasanitu mumafuna afe mwanyanayo, Lembani zomveka not atakomedwa simunati this is just de preaumber

  32. Let us wait en c sunday ndipatali anythng can happen or akhonza kuwonjezelanso another 1 week coz wangonena kuti abwela kuti tingodziwa kuti ali moyo other wise katsala kamodzi

  33. Let us wait en c sunday ndipatali anythng can happen or akhonza kuwonjezelanso another 1 week coz wangonena kuti abwela kuti tingodziwa kuti ali moyo other wise katsala kamodzi

  34. Pano mulibe manyadzi ndi nkhani zabodza zomwe mmatiudza zija? Ukati anakomedwa umafuna asamayende ndi banbo ako? Ana anjoka inu mwachita manyadzi

  35. kod amalawi bwanji tadzukani stop dreaming start driving. mukut palibe chomwe wachita ku dela lanu mukufna adzamange nyumba pakwanu nanga MP wanu alikut? mukafunse ameneyo za chitukuko.mudadzolowela kuthandizidwa basi pangani zanu. ngat mudakwatla cmudakwatlile president ndiye ngat zikuvuna kusamala zanu izo .pezani zochita anthu akusaweluzika ngat inu

  36. Ambuye Mulungu dalitsani mtsogoleri wathu Peter Mutharika ndipo mumpatse moyo wautali. Ndiziwa mtsogoleri aliyense mumayika pa mpando ndinu. Lolani kuti alamulire mpaka amalize nthawi yomwe inu Mulungu Atate munakonza osati anthu anthu amusogoze inu musanafune. AMEN!

  37. Kodi popita ananena kt akupita ku holiday? ife tikudziwa kt amakapanga attend UNGA , musapezelepo advantage kt alikuholiday kungonena chilungamo mzomwe iwe akuchita,philipi bisiness WA MBC ALIKONKO TIPATSENI FEED BACK YA PRESIDENT PA M,B,C.

  38. Zakuwawanitu popeza munafuna atafa hehe muyamba ndinu , Mzanu mumufunile imfa osamufunila moyo wautali bwanji? Akomedwako ndi chani Ku US, ngati ndi mulendo kumeneko amzanu akulila komko kuja mkukalamba ka mutha kukomedwa ndinu mwankhaula ng’oooooooooo

  39. Zonse ndinthawi pano anthu tikutukwanana ndizamziko zazii chifukwa cholambira anthu opanda pake omwe azafanso kma izafika nthawi yomwe aliense azazigugude pachifuwa mkumati oyenera kumulambira uja suyu nanga moyo wanga uja umatamanda anthu opanda pake aja bwanji lero ndkupita kumoto apa.

  40. Mayazi akugwiranitu. Paja munafalitsa kuti President wamwalira. Be careful, our life is controlled by God! Really devil is a liar..

  41. MUNENANENA MUTOPA KOMAA APM ALIPO,ENANU MKULIRA NDIYESIMUNATI,MAIYUSOABWELE TIMUMANGE.PALIBEZOMUNYENGELERA,MPAKAMALOKO ANATSEGULAAJA ATAWATSEKA,KASAMBALA SANGAZUZIKE EKHA,MWINI CASHGATEYOALIPO ABWELETIMUMANGE HULEAMENEYU,

  42. Hello friends, my name is Samuel Lughano this article contains a testimony of how i got cure fully from HIV/AIDS, i was diagnose with HIV/AIDS 4years ago, i contacted a doctor who later gave me some treatment, but it was like the treatment he gave to me were not enough i was desperately in need of something that will get rid of the deadly virus from my body, my life was miserable i lost my job and few of my friends, not quit long a faithful friend of mine came to me one afternoon telling about what she saw on net a testimony of how doctor olumo cured people from various kind of virus including HIV/AIDS, i was like this is bullshit that its a scam, but she old me she believe in what she had read on line’ she told me she will contact doctor olumo on my behalf and she did so, after some days she receive a parcel containing doctor olumo herbal remedy, she present it before me to use it, that when am cured i should pay back the money it cost her while negotiating for the medicine, after taking the medicine for some days according to doctor olumo instruction, then i decided to go for check up and i was happy to see that no sign of the virus was found in my body, i am very thankful to my friend, if you are having a similar problem or you need his help you can reach him on ([email protected]) or you can call or chat with him on whattsapp through +2348138956767, please share to save life.

  43. A PRESEDENT MUKABWERA ANTHU AZAKULANDILANI MWAUNYINJI CHIFUKWA ANTHU ANAYAMBA BODZA AMVEKERE APRESEDENT AMWALIRA , ENA AKUDWALA KAYAKAYA ZONENA ZIMACHULUKA, AZIPANI ZOSUSA AMAKONZEKELATU AZAGWILIZILESO KAWIRI ABESO NDLAMA ZABOMA

  44. Anapita. Kwao paja 2 si wakumalawi kuno 2 bwanji (bakili) amati apita amantha masiku atatu amene uja amaganizila kumene anabadwila nde inu mukuti anakomedwa pena mukuti uza kut amadwala amesa m’tudu umenewu umati unachokela ku tsulo cha njanje kd chitsulo chimadwalaso…km…mwanena kt anakomedwako kapena 2 kuli mahule kuposa kwanthu kuno kkk

  45. Lol mkanakodwa mkanapexeka nawo tsikulimeneli ku airport komweko mkasimikizedi kut ndi peter muthalika or ghost muthalika? lol kkkkkkkk kkkkkkkk kapena auka kwakufa ngat yesu kkkkkk ok any way welcome back Mr President koma akabwelamo atiuzo zomwe apanga ku America ko coz aonga ndalama ya boma yambili !! ndi ma overstayed awowo.wosokonekela apezeka tsopano,wakufa wauka ngat yili comedy ikhoza kukhala comedy of month kkkkkkk

  46. Kodi ku America ko sikunapite mtola nkhani woti aka nama wafotokozera a Malawi zimene Zimachitika kumeneko? Kungoti ziiii pa Radio yanu IJA.

  47. Akafikile kuyankha mulandu anali kuti ka green id kaja kakugwilabe ntchito akungofuna kuba ndalama zina apitenso akazisiyenso komweko analiko

  48. kodi president wathu abwera ali moyo kapena mtembo? the announcement is too brief! why??? Tikuyenera kuchenjera a Malawi, ndaletu ndizovuta. wait until Sunday 1:00 pm pliz.

  49. mayoooooooooooooo ine mwati chan satana akubwelaso ooooh my God mwalolelanji munthu opanda manoyu abwelenso,bolan akana pita bas ndidzina lake la Peter aliyikaso dziko pamotoyu

  50. I dont hav anything to say about this but to b honest this president will ruin malawians lives but anyway lets leave everything in god hands

  51. Malawi 24 ndi chatt cha miseche,mudalemba zoti TB josua mwakt ndipo afa,lero mukulemba izi,ndidamupepha Atate wanga mwachete koma ndavina kumva zakuchira kwake and tonse mwa ife akumwera timadandaula kut heee bwanjinso,zoona mpando akhalepo chilima wapakati?..aaaa sizikadayenda koma pano kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk ndamunyadira kwambiri.Mulungu dalisani Malawi,ndi sogoleri wathu.Ameen

  52. Guys this is bullshit mutiuza zingati eeeh wamwalira eeeh wadzuka, go to hell with your news kusowa zonena eti makape, mills for grinding lies

  53. amuthalika ñgati mwatopa apatseni ena mpandowo palibetso chomwe ife a malawi tikuwonapo mavuto okhaokha bolà kukhala wopanda tsogoleli

  54. Inu amalawi 39 ndichifukwa chiyani kubwera kwa achikulirewa mwalemba chichewa?
    Yet mayiko akunja akatumiza dollar kuti tigawane mmalawi muno aliyense azigulila chimanga chake mumalemba chingelezi y?

  55. Aa sabwere ameneyo azikhala komko kuno tazolowela kukhala amasiye kukhala mumdima kukhala opanda madzi akabweramo timpilikitsa

  56. Fupa lokakamiza limaswa m’mphika , akuluwa mwaiwowa munalibemo utsogoleri anangokakamiza pofuna kutchuka, don’t u see this guy is poor in mind? If he had leadership qualities he wouldn’t do this. dela lakwathu palibe wachita muutsogoleri wake mkuluyi pachimenechi watitayila nthawi ameneyu.

    1. Plz guys understand my point or else read it again, i didn’t say am happy ndi imfa ya munthuyu and i didn’t mention any word yokhudza imfa so plz chonde musandiike mau m’nkamwa chonde ine ndangofotokoza za mavuto amunthuyu kut palibe chaphindu ndikuchiwona muutsogoleri wake maka m’dela lakwathu mwina inu kwanu anakukumbukila.

    2. he z not politician even guys bt because of our ignorance if l remember well when iwaz young its only his brother who was participate on politics cause adali ndi chipan thawi imeneyo.we understanding that ur professor koma nzelu za u tsogoleli mulibe man musamatengele kuti chifukwa brother wanga walamulapo ineso nditha kukwanitsa mayaxi

    3. Kkkkkkkk u r really talking like a man now and I do agree with u Makanga coz it’s absolutely true. Now u r reminding me nkasa’s song ija amati ‘kuchipinda kwanga achimwene musazalowe ngakhale zitavuta motani …..musaiwale ndine mkulu wanu zamulemekezeni mulamu wanu kkkkkkkk I like it .

    4. umafuna akumangile nyumba kwanuko?Work hard osamadalira kwambiri dziko ndi lokondera,Peter u president wayamba 2014,so nde kuti ngati kwanuko kulibe chitukuko vuto ndi ma president oyambilirawo,so he cant fix evrythng overnight

    5. Ase Ine siwandale koma kunena zoona akuluwa ndiadyera ndi misonkho yathu and cholinga chake ndikugwetsa dziko basi, taonani eni nthaka akuthawila kunja ena opanda passport mkomwe sinanga ndiyodula sangakwanitse yet they r well educated, zimandiwawatu akamadya misonkho ya amphawi .

    6. Esther plz understand my points well , sindikunyozapo munthu mumfundo zanga ndie zoyambana ine toto plus kuyambana ndimkazi ngati iwe ndimazinva kupelewela nzeru, sindikukuletsa kunyoza ayi koma ndangoti uziwe kuti sindipitiliza kukuyankha, coz ine ndikunena zofooka za bwana wankulu iwe ukunyoza ine pomwe sitinayambane.

  57. Mulibwino ndinu mukukamba za azisogoleli ine ndiye ndikupita kukalima chizulo chifukwa zandalezo sindinazilawepo kaya zimakoma bwanji?

  58. Tikankhala ife nde kunva kuti akubbwela chimwemwe tsaya.

  59. ndikutha kuona kamuzu international airport ikuchepa Sunday likubwerari chifukwatu ndie kudzakhala mwana wamunthu pokalandira moya wathuwathu 2019 bomaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa!ana mwachepa

  60. Comwe mudziwe ndicoti olenga ndi Allah othandiza ndi Allah osati apulezidenti palibe comwe mungapindure dalirani Allah Ali ndi zonse

  61. Koma a #Malawi_24 mwasowa nkhani zolemba? Kodi chachilendo pamenepa ndichiyani? kodi simmadziwa zoti #President amakhala ndi #Holiday ya pa chaka? Anatenga #Holiday yake ndipo anapita kukapuma e eeee koma abale a #Malawi fe ndichani koma?

  62. Zopusa zianthu izi zopanda nzeru . Munthu zoona ndikumanyadira kuti nsogoleri wake wamwalira? Lero manyazi bwanji? Cela bonke amangidwe amaganizo opusawa torho .

  63. Tlibe nawo ntchito ameneyo…iye amaona ngat kwa merica stmafnako..akamabwela txemphana munseu nane ndkhala ndri on my way to komweko..Wiz khalifa wanditana

    1. Iwe wako ndiwa mulichelo usiku eti musamapange choncho he is our president till 2019 amene mukuwafuna kuti akhale pampandopo adikile 2019yo komanso adzalimbe osangoti ndabwela lelo ndikufuna mpando bwino bwinotuuuu!.

  64. Malawi sazathekanso ndithu! basi nkhani ikhale ya muthalika? iyeyo ndendani? akuti president koma palibe chanzeru akuchita kuntundu wa amalawife. Munthu akusiya dziko lake kukakhala kunja chonsecho ndi President nde ife tiziti chani? can’t you see that is trying to run away some issues? ndilankhulenso ndi inu mulipambuyo pa President wachikhalidwe chonyasayu. kuona mumaona kuti akulakwisa koma kumaombela mmanja mmalo mokoza zolakwikazo. muthalika wina ndi uja anapita uja wina ndi uyu, kodi mukundiuza kuti anthu anzeru kumalawi kuno anatha koma a muthalika basi??. Mukupezelanji fano chonsecho MULUNGU mukumuziwa?. Ngati ndalakwisa mundimange!!!!

    1. sunalakwitse baba anthu akulira magesi magesi chipresident chili duu kunjakoo fisi weniweni we will not stop until he go back to US and continue his surmit and bad wishes shall continue upon him self

    2. u must ask ur bitch wat does it means when they say #smartboy. then wll stop comment stupidity like this. #ubani_wena

    3. Nosense @ Louis Yonasi and I can see that you are the one so stupid and mbuli yopanda ntchito. Please ask your bitch too the meaning of Yonasi! nosense!

  65. Wachedwakale,ndiyemkumasoabwelapasabata; Mafuso, Kodiamataninthawiyoseyi? Kodiamagwilitsantchitondalamazakekapenazaboma?Nangawaonongandalamazingati? Ndimtsogolewadzikolitiamenewakhalanthawiyaitalingatiiyeyu?…Mzovetsachisoni Dzikolosaukangati Malawi Mkumalidyelandalamazamisonkho.

  66. Jafalie manyadzi mulibe,mumati muthalika wafa lero mwayambanso kunena zina,devil is ugly indeed,ife kunyadila kuti Mulungu wamva mapemphero athu,President wathu akubwera wa moyo atalengedzedwa kuti wamwalira.Thank you JESUS…

    1. Our president is alive baba,coz death is not his portion,no weapon formed against him shall prosper.In JESUS Mighty Name,Amene mumaganiza kuti Peter wamwalira pepani kuti zinthu sidzili choncho,komanso uthenga wapadera ndi oti samwalira nsanga mpaka Yesu adzabwera..Amen

    2. We don’t have the power of killing someone if we only ganiza of killing we have killed nde remember that in the holy book welcome back mr president

    3. linda madzi apite ndiye uziti ndadala, tiyeni tidikire afike wamoyo ndiye tiziti tadala, kwapita Presdent kumakhala ma camera man, koma uku kokha kukudabwitsa. Tiyeni tikhale chete kuti madzi akapita ife tidale.

    4. Tambala oiwala khola lake kukalowa la eni zamanyazi kuchita kumangidwa chingwe kuti tiyeni mavuto momwe alili m,malawiwa ine ndye zandinyasa vote yanga inapita madzi basi

    5. Inu amene mumalemba tsamba ili nonse ndinu zitsiru ndithu mesa mmati a president amwalira lero mukuti he is coming sunday you must be very very careful with your up date otherwise u gona dance unsung song.Mind u.

  67. Am hap to hear dat anthu oipa anali bsy kufalitsa zot mr president amwalira usatana kuipa mtima its nat gud ladies n gentlemen long live mr president

  68. Munthuyu anamangidwa mwachinsisi ndi boma la america.Iye anadya ndalama yokopele anthu kuti azikwatilana ofanana ziwalo.Mutharika analephera kukopa a malawi kuti kuti alowe nawo munchitidwewo.Mmalo mwake iye anawononga ndalama yomwe anapasidwa ndi america yomwe inayenela kukopela anthu.Boma la America linangokonzeka kuti, Mutharika akazapita kumeneko azamumange.Ndiye tsoka ilo ulendo wakumtsonkhano ndi omwe anamugwira ndikumukwizinga unyolo ndikugwila kalavula gaga kwa 2 weeks.And panopa Mutharika walonjeza boma la America kuti a yesesa kukopanso anthu ndipo akhala ndi njila zokopele anthu.Zambiri timva akafika kuno kumudzi.

  69. aaaaaah amene anali akuyakhula za APM wasenza ndowa nd MALAWI24 nde pano mukut al moyo ……. mau anga kwa mutsongoler wanga nd awa asawabwenzere choipa a oppsition nd enao angot mulungu awakhulukre pa zomwe amanenazo …..ena pano munayamba kumumema VC PRESIDENT asithe chpan cholnga mudyeso nae …..zakukanikan …..mulungu ampasa moyo wautali ….. iweo ufa kma APM sadzafa akubwera kukhala chete sikupusa ai….. amafuna amve zomwe munganene inu agalu inu osadziwa kuyakhula lomwe

  70. A dpp musakomedwe chifukwa mukuluyu sabwera monga analili kale. Ziwalo zina azisiya ku America. Mwina simuzamumvaso akuyankhula.

    1. Mulungu amakondadi wina aliyense koma amasiyanitsa makondedwe ake. Nchifukwa chake pamapezeka anthu ena amwayi ena atsoka. Ena olemera ena osauka. Ena ophunzira ena osaphunzira. Ena ali ndima private jet ana or nsapato alibe.

  71. Its better to stay hre en calld afreghner,than to be their in malawi en surfering for ever thng,malawi saza tukukaso thaw yazmenezo inatha.

    1. Abakhaxo nde ati kodi…..makolo anu kukutumizani ku xool inu kumati iyayi tikupita ku Joni nde tawonani manyi mwalemba apawa…….ngati zakuwawa undipeze ku cosmo city

    2. Mbuzi za anthu mfanz ku joniko olo akugona pamulu koma akupanga cash potha pamwenzi ndalama yoti olo wa police wa ku malawi sangalandire olo phunzitsi sangaipeze ku joni vep siisowa pamene kumalawi mapepala amaolera nyumba

    3. Mickhy, and Andrew, mbuzi zosayendazi mukazitsanza akupakan i ubongwe… Agalu awa palibe chanzeru akulankhula. Mwezi ukamatha kuMalawi kuno nkhawa muntima pafupi kudzimanga chifukwa changongole. No…sence agalu ngati awa plan inathera ku Malawi…Congrats guyz.

  72. Sekulu tamabwelani mavutowa tizizawawonela limozi osti kumangotasa uko udindo mumafuna uja ndi umenewo osawuthawa pano

  73. Kodi malawi24 ndi munthu kapena kompyuta?ukapanga post sikuti uzingowasiya anthu azingokomenta okha hop ukuziwa bwino komwe kudali peter nde wati adakomedwa?ndi chan?umanama kuti wamwalira ukuziwa kuti akukomedwa?shaaaaa koma mdubs sizatheka mwaputa dala sidine azafikilatu kutukwana ohoooo ine zisandikhuze

    1. Kikik yah nyimbo yaBilly Kaunda. Mulandileni mwana yo . Watenga gawo lake lachuma oh. Chuma chose chija waononga oh. Munyumba yaatate anga zakudya ziliko zambili nanga ine ndivutikiranji kumadya mapizza. Ndipita kuMalawi akandilandira.

  74. Why don’t concentrate in development stories bt u are busy with 1 person who behave en hav some mistakes like u Munthalika is still president till 2019

    1. …. how can you feel if i say that to your father, brother of child……? what will you gain over his death..? will your all troubles and problems disappear coz of his death..? even mulungu amene samakondwa ndi imfa yaochimwa coz ilibe chipulumutso, then iwe ukuipezakuti mphamvu yomakondwera ndi imfa yamunthu…? you, me, Peter and all malawians we’re all sinners, it’s only that we sin differently, and if munthalika’s sins are nor similar to yours, that doesn’t make you an angel,…! Remember no sin is greater than other…….., funeral is not entertainment, its a loss of life, the separation of body and soul and its a tearful moment for relativies and friends…..flush that sprit out of your mind, osamakhala ndimtima wausiku, ufiti umadzetsa umphawi…. grow up man, inotu ndinthawi yachitukuko osati yaumbuli…….

    2. U man if the catch u and send u at court, are u sure to say that in front of judge? Sometimes u must have respect. Even the bible said that respect to the country leaders

    3. Eti, eti, eti, ife tinakondwera kale and we thought thngs wud move forward. Nw that he is coming alive, mayo ine! Pliz dont come alive!

    4. kkkkk ndibwino kulola Peter apite kumanda bas olo baibo linanenso kale kut ndibwino kuchotsa chinthu choola chomwe chimaononga zinthu zambiri,so its good peter apite rather than anthu azivutika chifukwa chamu2 yu modzi uyu.

    5. Nanuxo anthu omabakila zitsilu ndnu amene mukuononga dzikoli nthawi ya david atapha goliat mexa anthu anasangalala why .umbuli ndiomwe wakula apa .ife tikufuna chilima anatisamala buino m’mene amene mumati peter anali kuthawa ma blackouts

    6. Nanuxo anthu omabakila zitsilu ndnu amene mukuononga dzikoli nthawi ya david atapha goliat mexa anthu anasangalala why .umbuli ndiomwe wakula apa .ife tikufuna chilima anatisamala buino m’mene amene mumati peter anali kuthawa ma blackouts

    1. Ndindani amene amanena kuti wamwalira,ndindaniso amene akunena kuti sanamwalile akubwera weekend.mwiniwake wanena kuti akubwera a peter wo

Comments are closed.