Ndende ikudikila anthu onse amene akufalitsa nkhani yoti mtsogoleri wa dziko lino, a Peter Mutharika, akudwala mwakayakaya mu dziko la Amereka.
Malingana ndi nduna yofalitsa nkhani imenenso ili mneneri wa boma, mtsogoleri wa dziko lino’yi amene anapita ku dziko la Amereka ku msonkhano waukulu wa maiko onse ali bwino ndipo ndi wathanzi.
Izi zi kusiyana ndi malipoti ena amene anatchuka oti a Mutharika akuonela pakhosi ndipo tsiku lina lilironse anthu atha kulandila uthenga wa chisoni.
A boma anenetsa kuti a Mutharika sali mwa kayakaya ndipo anthu onse otchukitsa zimenezo ndi ana a Satana chabe amene amadya bodza.
“Nkhani zoti a Mutharika akudwala ndi bodza la mkunkhuniza, zilubwe ndipo ndi bodza lochititsa nseru kwabasi,” afotokoza chotelo a Ndau mu kalata imene alemba yopita ka mtundu wa a Malawi.
“Tikufuna tikumbutse a Malawi kuti ife a boma tinanena kale kuti a Mutharika akugwila ntchito zina ku dziko la Amereka,” apitiliza motelo a Ndau.
A Ndau aonjezelapo kuchenjeza anthu onse kuti boma silinyengelela koma kutengela ku khoti a kapilikoni onse amene akutchukitsa zoti mtsogoleri wa dziko lino watsala madzi amodzi ati poti uwu ndi mlandu malingana ndi malamulo a dziko la Malawi.
“Kutchukitsa nkhani ya bodza yokhudzana ndi umoyo wa mtsogoleri wa dziko ndi mlandu waukulu oti munthu amayenela kumangidwa nawo,” atero a Ndau.
boma liyenela kumakamba zoona,munayambala kale kutipusitsa.kodi mubisa mpaka liti?
Ido’nt care that petter he passed away that’s good komaso tilibe nazo chito zachita bwino amatikwana ufumu wa u pressdent amasiirana ngati nsima mumbale za ugalu komatso ndima foregner ameneo si ma citixen ayi… Ngati kwaoko aliposo wina mene wafa pitalayo alowe naye afetso asiye ufumu umeneo azausiya after kutha utundu wao onse nafe sitilola kulowetsa wina unless atata anthu onse ku famlly imeneyo agalu ameneo
chilungamo chikukusowani nenani zowona amutharika alikuti?
Amangeni agaluwa zopusa basi wamwalira NDE chani?
Mavotinso mukapasidwa simawina ndiye mukhala mukupha atsogoleri mpaka liti?
Chafa basi tipume ife manxi pano ndi week ana anthu akurephera kupita ku school kamba kamanxi nd mages kkkkkkkkkk Ine ayi kachitayeni basi
Ndipezeni ine kuno basi ngati family yanga yanena kuti James jailosi banda wamwalila amene angasuse ndindani bwelani kuno munditenge ineyo basi xanu izo nokha bomamo wapita basi
Nde ufumuwo amusiila ndani?
Kaya akudwala kaya wamwalira,zonse timamva kwa inu,nde ayambe kaye kumanga inu then malawi yonse
Kumangidwa kwa chani?utsi sufuka popanda moto,ause basi
Ndidolo ameneyo sanga duwe mwina akuthima kaye zibawa ndioba
Abwele basi
That Only Shows How Fully Corrupt U r. Stupid Cabinet, Mbuuzz! Agaalu! Agwenywengwe! Ananchidwi! Foolish. Oooo Why My Homeland? Why U Make U Regrate T b Born Malawins?
Oky tamva sitinenaso koma ali………… ………
Kufa mofanana
Koma kumalawi kuno anthu ndinu vitsiru ndithu bansi busy kumakamba nkhani zopusa pa fb m’malo momaganiza za tsogolo lanu mukufuna akuwonereni ndi ndani dzimitu zanu nonse amene mukuti mukakhuta iwisa wanu/white star pajonipo mkumafalitsa mabodza musamale napo pakamwa panupo mungadzitanire mavuto panyapanu nonse mudzatipeza kumalawi kuno mukudzitenga ngati madolo muli makape mukabwera kuno mumakhala opanda kalikonse anthu ovetsa zisoni inu ulesi basi kusowa plan yopezela makwacha pa m’panje pano zitsiru inu.
Pita Muthalika Akanakhala Kt Sanatisiye Akanayakha Kut Ndilip Ndakhala Ndikunena Thaw Ndithawi Kut Johntembo Ndi Muthu Oipa Kwabasi
Komande
OK mangani koma mumange aliyense coz it was a song for everyone. Anthu opusa inu. Ziliponso zoopsyezana? Mangani tonsefe, za ziiiiiii tiyeni uko.
Ngati mmamva misala ndiyomweyo. Mwasowa zochita kani? Mukutchula zomanga anthu just becouse akulengezesa nkhani imeneyo, maliro amabisa? Bwanji simuna mange anthu omwe anaononga miyoyo ya alubino? Anthu oipa inu ndiosowa chirungamo kagwereni ukoooo
anamwalila munthu mukumanga anthu chifukwachani? chilungamo chimakukanikani eti
one of they”i think it’s you stupid pple and peter mthalika hi’s very stupid again. ali ndichani ife timazisamala panya pake msogoleriyo umuuze.
one of they”i think it’s you stupid pple and peter mthalika hi’s very stupid again. ali ndichani ife timazisamala panya pake msogoleriyo umuuze.
Olo ataduwa Malawi akhala ndi president wina mukukhala ngati amatigulira ufa bwanji kukhala moyo kapena kumwalira it’s a life reality as simple as that
ZOWONA AMANGENI AMENEWO AZOLOWELA
Zoona wamwalila omangidwa akhala amene akuononga chuma cha boma
Malawi plz this is not 1914 if the government they refuse what the people said then put me president on the network tv s tiwawone kusiyana ndikuti kwawophyeza anthu ndikuwamanga so if it true that mr presented he passed away who can rest you ???????????????????
Nanga Ali kuti osayankha ekha kuti amene akufalitsa nkhaniyi achite manyazi.
Kaya wafa zake izo ndikandaniso kameneko kachita chani kuntundu wa a Malawi kumanda kwayasamula basi
Afa kumene
wanyala
Kkkkkkkkkkk ine ndiseke kaye kumangidwa kkkkkkkkkkk tsitsi chani pali khani yomangilana apa Aaaaaaa RIP
Palibe nkhani yophyati xachitika zachika apa ifeso makolo athu anamwalila balibe wamuyaya ndamali heso awa kayandikumanga amange odiodi kundata bashale. Tikakumana konko wapita ndingongole yanga. ishlah
Aaaaaa akamange agogo ake iyaa amange ndan
Kaya amwalire tonse TIZAFA TIZALISIYA DZIKO…SO PLEASE PETER MUZIMU WAKO UWUSE MTENDERE… AMEN
Nde mumanga ambiri2
Kodi vuto la zachuma lidatha m’boma kuti muzikasamalira anthu omwe ali ndi manyumba awo,zakudya zawo..only because anena kuti a president amwalira? If it is not true then that is their opinion but the president is alive! If you are clever enough to care for Malawians, that can not be an option! Muziganiza inu!
Ndikumuona apayu not Peter mutharika this is robot is looking like mutharika.
The nothing like arresting them ! For what ? Africans r well known in misusing their smartphones coz others just joined Facebook, instagram, twitter, watsap etc some few days ago. Let them get used to it and leave them have freedom of speech.
Iweyo ndi mtalikayo ndinuopusa
Kkkkkkk koma zinazi ukamva
Kkkkkkkkk kapena wadzuka pano
Zachamba ngati ife tingadandaureponso! Mwinanso magesi abwerela pakare paja
Zimenezo akauze omwe savota momga aMBONI_ZAYEHOVA koma wosati ngati ine,ndizisekelera munthu akundionongera msonkho woti ukanathandiza munthu wina kupeza moyo wabwino pamene iyeyo akuseweletsa
Rest in peace pitala. Namathanyula
Amangidwe abodzawonse
Kkkkkkkkkkkkkkkkkk zoona ndiva za mbiri apa
Mmafalitsa nkhani ndinu @ Malawi 24,munatiuza ndinu,mmangidwa nokha
Ayamba kumangidwa ndi myeyo chifukwa wapwanya lamulo laboma zaziiiii
Ngakhale atamwalira ife tilibe naye ntchito angadandaule ndi agalu anzake angoononga ndalama zabomawo
Aaaaaaa iye ndi bambo wa ana ake ife tinamulemba ntchito pa may 20 kuti atitumikire osati kutinyodza..kapena kutibera misonkho yotukulira dziko lathu ayi..
Iyeyo ndi chitsiru chotheratu akutani kapena akusunga ndalama zaba iye kwathuko abwereko ..ngati wachedwa kuti samadwala akuyenera kulandira chilango.kodi mwaona kuti amalawi ndi oputsa kuti muzingowaopsedza ndi unyolo? wayambitsa maganizo oputsayo ndani ? ndimushute asatire malemuwo…pajatu mumkatero ndi Bingu Ethel chimodzimodzi koma lero onse ali m,manda tsono iye wapambana chani?
ladies and gents,don’t be surprised pliz, the president is there also looking fo green pastures just like more Malawians are going to other countries for the same reasons
Who ever came up with the idea is a retard,this will just increase the # of prisoners which in return will hurt the government itself so they better think of better ways of protecting information regarding the presidents well being
Siti kumufuna basi mesa mukati ndiwa school ndiwazelo kwambili bwanji sakupanga zotheka achoke kkkkkk
Umanga amayi ako
Anthu awa amaganiza ndife zitsilu zawo. Mphamvu za dziko la Malawi zili mmanja mwathu ngati watopa atiuze tithaso kulemba ntchoto president wina
Its non of our busness.
Nditeyetu amanga chigulu cha anthu
Amangidwe ndi fiti osakamba za maliro abambo wawo!
Ngati mukulira chocho nde kuti chamwaliradi basi awuze mwa ambuye…..ndimangeni ine pano ndi kandende kanuko
Tindende take zodzadza kaleti
Nanga alikuti?
Ife sitingaope kumangidwa ndipo nonse mukufalitsa zoti mumanga Anene akuti Peter wamwarira ndinu makape.ndipo ndizisilu. Osangonenachilungamo bwanji kuti watsamaya
Atilankhule ngati mufuna tisamanene.Kodi azitilamula Ali kunjako?
Wachita bwino wamwalira tibwerera kumalawi tsopano
Ananditaitsa nthawi yomubvotela
Kungomanga ine nde akuputa kumwalila zenizeni tsopano
Wafa basi zake zimenezo
Mmmmm za kale kale izi inu ndi phuma la DPP mmene mumawadziwira muja sanakabweza kale moto
kkkk kukhala mu malawi ndikulimba guyz moti zofunsana zatha sopano
Guyz dont judge like that peter he iz still alive end zot akudwara or he iz dead tht iz not true end lwill follow peter untill untill for ever.
Kkkkkkk ma prophet gwilani ntchito yanu pitala wawonjeza akufunika azikacheza kwa ambuye ife tione zina……watizunza mokwanila mpaka kuliwuza dziko lizidya makoswe ndi ziwala eish pokhapo ngat Ali moyo afe ndithu ngat wafaso chikakhale chikuni Chaka jahena
Zoona abale
Tidikila ndendeyo until choona chitadziwika koma tsopano loko atamwalira palibe film akuyenera kufa basi
Kaya wamwalira kaya alimoyo zake izo asova yekha aona kuti atani
Ngati angapezeke kuti wamwaliradi, maliro ake akayika akayidi
NDE tiope?
Ngat muli moyo kulikonse komwe muliko i hope mukuzinvera nokha zomwe mntundu wa aMalawife tikufuna..#WE #WANT U #BACK TO UR #COUNTRY..what kind of president r u ? zotsatira za izi zimabweretsa matsoka aakulu pamoyo wanu baba just come home n solve this issue…Kumalawi ndidziko lamntendere mumatero mtendere wake uli pati apa anthu akuvutika ndikumati dziko lamntendere !!!! we don’t want u dead we need u alive ngati kuli kuchoka pampando muzachokepo bwinobwino osati njira yake imeneyi ….
Umanga agogo ako
Zilipobe kumalawi zoopa munthu kumangidwa??? Ngati siukudwala kapena siudamwalile ukubisalilanji??? Zomwe umapanga ku America zidatha. Ulendo wa boma wasandutsa opanga zako???? Tuluka poyera anthu akuone
Big up my bro!
ndekuti azikhala life in prison kapena ayi.mwina enafe tingakaloweko timafuna life in prison
Nde onsewa mukwanitsa kuwamanga? zoonadi amalawi ndi Mbuzi zomwe amakonda kuweta. wapita wapita basi. ndikunenatu ku Americako.
amange kaye page inoyi then tiyambe kusaka anthuwoo mwaavaaa
Kodi atati wafadi nanga maliro ake azazikidwa kuti? Kumbukiran mau oti soka likalimba umaphwisa ndi mtembo anamalira ali cheteee. Timangeni
Komandiye okamanga ineyo2 akozeke.komaso sangakwanise kundimanga akulephera kumanga JB nzimayi what about mamuna ngati ine?Zachamba basi
We can say anything,we got freedom to talk, ungamange mtundu wakwana!
kodi mukabisa ndi kubwera mtembo mudzadya? auzeni zoona anthuwo osati kuopyezanako ai,mudakali ndimoyo wachikale ujabe?
nanga poti ndinaona pa BBC ENGLAND akuti mutharika conditional critical ndiye kuti muwamanganso ma announcer aju BBC wo nso?
Amangidwachifukwachayani?
kkkkkkkkkk zachamba et ndi mageni ine aperter alandire chibalo pasi achedwa kuziko laniake kkkkkk
?????
Lets jst wait n C the trueth will come out.Bisani matenda koma maliro tidzawadziwa.Mayb there bsy making Embaming first then then they will decrere
Bola mwina mukatimanga tizikakhala kowala bcoz kundendeko kuli ma sorah komanso ma generator…. Kusiya kuti tikhale kunjakuno koanda magetsi, madzi komanso no president aaaa
R.I.P mr president
Akumanganitu man Omar Nason musanene kuti wamwalira
Nangazikaululika kutiakudwaladi, kodi ifeyotikumangeni? Andaletikukudziwani kutiinuyo mukungofuna kukwanilitsa ntchitoyanu . Komamusaiwale kuti mawalino mukanyelelana mudzatiululila mongamonwe adaululila kaliyati. Kutiiyeyo ankawopa kuchotsedwa ntchito akavomelezanwachangu kuti bingu wamwalila. Zosezo adaulula dzitamunyela ndenanusi mudzatiuza .komaifeso linya tasamalakale potimwaiwokhala ndiwunyolo tilibe
kkkkk eekwanthukunoooo wakufa akuwopa kuwola 2016.
Anything like intimidation will not take u anywhere, even if u can say it in strong or right terms u are to get nothing, the only languege that Malawians can understand quickly is the the languege of extrim trueth, we want our presdent…..dead or alive
Kikikikiki poomanga munthuyo mukuti walakwa chani?
Ife tili kundende kale, mavuto ali kunjakuno ndichimodzimodzi nyapala akuseleza zaka 10.
Kkkkkkkkkkkkkkkkkk all the best bushiri our future president
Hello to everybody am very happy and glad to share this my wonderful and amazing testimony to the whole people of this world of the great work of DOCTOR dr sule an india doctor. This man is not a native doctor or a spiritual man, he is an herbal doctor that cure dangerous illness like; HIV/ AIDS,KIDNEY PROBLEM,HEART DISEASE,CANCER PROBLEM, and others dangerous illness which other english doctor has no solution to. The may reason why i am sharing this testimony is to tell the whole world that this india man DOCTOR //sule is here to help people who has that problem that are listed below.this india man is not a fraudter non a scammer because this man has help me and my wife after ten year of suffering from HIV/AIDS, he is a real good doctor, i and my wife was the one who told this DOCTOR //sule / to create an emai address because through this email he can help who has this problem. Truely this man is not a scammer he is a real doctor he is not here to eat money he is to help people because he has already help me and my wife. This india man has an email where you can contact. Pls d¶n’t play with this illness when you have it or someone around you. Contact he for he on his email address………. dr.sule via whatsaap +2348162447651
Kkkkkkk ineyo zingodiwaza chifukwa ndakumana nawo dzulo akuyenda wapansi
No stress ndende zilibe malo anthu onsewa akakhala tiyamba civo war tiyeni nazoo
Aise just come out and talk to the malawias coz they have missed you a lot ambuye what’s wrong with you ?just come out and sing your song ine ndilibe problem people they are waiting for you they want to dance with.
Musaopse anthu walamula zimenezo ndindani
Who is he?we had the lion of Malawi ,where is he?every body will test death.no matter how rich ur, no matter how power ur ,nobody will be forever.people just want to know the trueth
.is he ilive or not ?why are you hiding the trueth?is he wamuyaya kodi?
Matenda munthu umatha kubisa koma imfa sibisika remember the late Bingu
Chilima manga malamba tidye ndalama zaanthu adha aja avaya basi
A Malawi 24 news mukuopa kunena kuti president wamwalira koma ikanakhala nkhani ya kuluza kwa Big Bullets titaidziwa kusanache, just imagine munthu oti wapangidwa imbamu kale angakhale ndi moyo ?
Malawi sazatheka
wamwalira wamwalira palibexowamwalira wamwalira badewamwalira wamwalira basi palibe zomanga apa,ife tizama inu coz mwatichedwesera kt…….
ndege ya nyamula mtemboyo igwenso tisazaonenso nkhope RIP bwampini
Ngat wapita wapita ndidzina lake lomwe, palibe kubwera wamoyo, omangidwa ndi ambiri #R.I.P
Kaya amwalira kaya ayi nzakezo. Anza ose anabwelera mumayiko awo, iye bwa?? Anamwalira ndimangeni ine.
Eeeeeeeeh i will not put any comment, bcoz am afraid of being arrested…
#But_am_gree_with_you_all_guyz
Matenda bisani maliro tizamva
Ine ndikamangidwa ndidzatulutsidwe abwana akabwela
azanamiza antu kufika riti
lam the visitor of this group, mwati wamwalira? iyeyo sioyamba kumwalila brother wakeso anamwalira palibe zoopsezana apa ndanena ndanena
We are going to conduct anational wide demonstrations on friday.until the Government informs us about the whereabouts of the President and what he is doing.To unvel such things,its not democracy.
we are not saying that he is dead we are jst asuming that he is dead coz he is nowhere to be seen
we are not saying that he is dead we are jst asuming that he is dead coz he is nowhere to be seen
Onse obisa kuti President akudwala kapena wamwalira amangidwa.Apo ndiye palibe zokambirana,you will be in for it.we need to have information about our President no matter what.
They will manage?
Kkkkkkkk kujowa mikodzo ndi kukaponda manyi fundo yomangila mwana pamene kholo lake limodzi silikuwoneka asafunse basi walakwa awuzeni a dad amwana amulakhule watopa ndikufunila maso
Hello friends, am Juliet Phiri by name, i was one of those millions of people living with HIV, i received my breakthrough with the help of Dr Olumo whom i met through the testimony of someone he has helped, after some series of conversation with the person sharing the testimony i decided to contact Dr Olumo which i did, after some negotiation he sent me the medicine with an instruction on how to use it, i notice some change in my body when using the medicine, after completing the dose as instruct i went for test only to be confirm negative by the doctor after the result came out, words on the internet can not express it all, if you are in the same condition and you are looking for a way out of it you can contact Dr Olumo on his email address, [email protected], or you can call or whatsapp via +2348138956767.
Palibe zoti aopseze anthu kuti amene akufalisayo amangidwa never amene amalembayo wherever u r udziwe kuti palibe amene anga wope kuyankhula zomwe zamveka ngakhale mubise ngati zili zoona simudzapanga manyazi polengeza? Nanga zinatheka bwanji nduna zonse kubwela kusiya president yekha? Ndipo mapresident amaiko ena onse anabwelera mmakwawo nanga peter bwanji sakubwela ? Padziko lapansi palibe chinsisi tiyankhula zomwe tamva no one can stop us n we r not afraid
Malawians have the right to know where their president is. Just inform the nation then all this mess will be cleared Hon Minister
Kodi aboma mukudandaula cani munthuyu mkulu waketu anamukonzela kale malo ake
Anduna tiudzen president abwera lit kuno kumalawi?musatikulunge msalu kumanso mwayesa ife opusa
Mumpase suspend akabwera nanga kuchoka amachoka chotcho kungoti ndivaya kumsokhano,mwina wasala wawokha msokhanowo
Iwe amene ndamene ukulemba zoombanitsa mitu anthu
President wathu wamwalira iwe ukufuna utimange tizikalilira kundende zoona
A fokofu
Pamapeto a zokambilanazi tiyeni tizuse chikhomo chathu “Luciuos Banda atiyankhule “ulemu wanu bwana 5 mns ur speach!!
ndizoona palibe kumanga munthu apa wamfabe nanga sakubwerera kwawo bwa mukubisa nthembowo. ndiye mugawanetu mmmmmmm mungatani oro mutani wapita ameneyo ause munthendere ame
Mkukana chilungamo zimenezo ndizoona
Ndende mukati Mwa ndende, hahahaha, are u calling it malawi or maula prison?
kaya chilungamo chidzadziwika chokha.
Wapita Wapita Basi Kodi Kutimangako Kumupatsa Moyo Wautali Kuuzimuko? Anduna Imeneyo Ndiyo Dimocracyi
Zovuzedi ha
Pathu zipadziko tingopitira, one day anyone will go no matter a position he holds in the society
Kukhala 5 million ku ndende
One thing you should know is that whether he is alive or dead is none of my business. What matters is that am worrying about my tax money because I pay PAYEE and everything that I buy is taxable too. So do you expect me to give it a smile? Shame on you GVT mouth piece
Timangenitu
She’s never been to Malawi, but she really wants to. Ellen Bickle
GOD plz take him
Yambani kumanga ine muone
Gidesi Chalamwamba.kkk ft America.
Will be released when he dies,thats the jail term,God have mercy
WALEMBAWE NDIWE CHITSILU, KOMANSO MUTHARIKA WANUYO, KOMANSO AMENE ANGATUMIDWEYO NDI CHITSILUNSO.
YAMBANI KUMANGA INE ANTHU OPUSA INU, KULAMULILA KWAKUKANIKANI SHUPITI ZANU.
somewhere or nowhere, died or alive tilibe nazo ntchito komanso mantha chifukwa ndi president wopanda masomphenya. useless goat! ingobwelesani ntembowo tikataye kundata ife! kkkkk
Bomaso pena ndi ropusa kwambiri gyz mukubisa chifukwa chachiyani osangorengeza bwanji kt Peter wafa muchita kukhara ngati kt akafa iyeyo akatseka manda bwanji aa zopusa
Zanu izo Chamoyo china chili chonse chizalawa imfa,,,Malembo akutelo…
Ineyo nimangidwe km Peter akudwara mwakakaya komaso chimene mwapangira pack magarimoto a DPP ndichiyani kuti asayende mwapanga ximexo chifukwa chiyani sinidxarora ntundu wakwamereka udxaramurireso dxiko rathu ta its better utarowa ung’onoung’ono ndipo ameneyo afe tiribe naye tchito ngati kuti adawina chirungamo . mukanifuna muniimbire 4ni pa # iyi 0710590223 ndiri kuno ku JHG
Hahahaha kkkkkkkk Koma iwe !
Koma amalawi sibwino choncho kumanama kuti mutsogoleli wadziko (kuti wamwalila ). Mutsogoleliyu aliponditu ngakale mutavafuntsa aNdau akuuzani zoona. A Ndau akuti a APM alipo ku American kugwira nchito zaboma. Its only that kunoku magetsi kulibe sitingate kumuona mutsogoleliyo paDSTV kkkkkkkkkkkk koma ine kkkkkkkkkkkk basi ndalekela pompo trump woyeeee Hillary Clinton woyeeee kkkkkkkkkkkk
Peter ndmuvumbwa akukakamila bwanji dziko la eni pomwe dziko lake lilipamavuto ndeakamankhala kumeneko nanga ndindan ataliendese dziko nde bac zikungofanana kut wamwalira
Poyamba mukawamange madotolo amene alephera kupulumutsa moyowo kenako tonsefe maliro amenewo adzadziika mmanda okha tonse tili kundende
NGATI SANAMWALILE AI EISHHHHHH AKUCHEDWA PLZ ENAFE MOENDA MUNO MWATOPESA
Zowona
Maguyz Anthu Azasiya Kuyankhula Pokhapokha Atamva Kt Abwela,kupanda Apo Zoyankhula Anthufe Stileka.Cifkwa Skt Ndtopola Ayi! Koma Tikufna Mnthuwa2 Abwelele Kuno Kwawo Aziza Ptlza Ntchito.Ciliconse Cayma Cifkwa Caiyeyo.
Maguyz Anthu Azasiya Kuyankhula Pokhapokha Atamva Kt Abwela,kupanda Apo Zoyankhula Anthufe Stileka.Cifkwa Skt Ndtopola Ayi! Koma Tikufna Mnthuwa2 Abwelele Kuno Kwawo Aziza Ptlza Ntchito.
Anthu Opanda Chifundo Ngati Inu Sindinakuoneni Zoona Kumachita Kufalitsa Ngati Mpila Wanyasa Big Bullets Ndi Beforwa Wanderers Mwana Wamzako Choncho? Ai Ndithu Mulungu Akuoneni Inuyo Mwapadeladela Mwamvatu? Ine Mwandikwiyitsa Kwabasi. Nanunso Ngatidi Mulibwino Tabwelanitu Ifetu Umasiyewu Ukuti Wawa Ife Tizivutika Ngati Tilibe Bambo Wathu Muno? Magetsi, Madzi, Komanso Ine Malipilo Anga Sindinalandile Akudikila Inu Dad.
Kufa ndi kufa and death itself is never reversed
Naai
simple! bring bak da lyts then u gonna R.I.P.(rest in pu……)
Koma Guyz Akungowophweza Kt Ticite Mantha.Koma Funso Ndkt Kod Iyeyo Ukutan Ku Americako! Popeza Azake Onse Adabwelako? Ifeyo Tikungofna Kudziwa Cilungamo Bas.
Za usuku basi,ndi mulungu bwampiniyo?nanga alikuti?akutha ndalama za boma kumeneko,apo ziii amwalira ngat nchimwene wake amemeyi
Muwaziwa bwanj
Eish guys i will send de angel to finish dat magogo!am crying for our national hiiiiii
Akudikila kuti Escom ikonze mablack out ali mdziko munowa.
Uchitsilu Eti? Ukungolakhula Kufuna Ndalama Eti Malamulo Umadziwa Iwe?Ungamatiopseze Presdent Ndiwammyumbamwako?Ndisamvemso Pakamwa Poolapo Pakunukhamso Ungotiuza Kuti Akupeza Bwanji
Muyambe ine coz am 1 of them
Wafe plz pumbwayi
true or false? musova
This bastard presdent he is doing like street kid . Indeed he is useless doing fokolo . I cn do better than him. Guys we hv to do something be for things come worse. Since our hero hk banda rul this country wasnt happen . Look our currency going down each n every hour. Kids walking no shoes n sleep empty storch our patents failing to pay school fees. Guys wen wil stop beg from out country?
zimenezo nde zopusa osamanga anthu amene akuba ndalama zaboma ali ku America amanga ndan ngati alimoyo kapena akupuma mwathanzi bwanji osayankhulako komwe aliko kur anthu kuno kumudzi tidziwe zoona ngat asowa ntchito apolice ndibwino apemphe holiday akalime kumudzi
tikadziwa kut peter simalawi kwao ndi kwa amereca ndiye asabweleso komaso akachita zamasewela akufad alondola m bale wake ine atafa peter ndikhoza uchita sadaka chifukwa watizuza itini vote ndiyathu mot afe ndithu
Minister akuwopa kuchotsedwa ntchito nde tibadikira mwatchela ku America amalawi tawona ….
RIP pitala
Koma sopano chimene chikukhalila iye kudziko lawen nchan?? Akungoononga ndalama zaboma ndizopanda pakeeee ma billion a ma kwacha amene akuononga kumeneko pamene ife amene tinamusankha kumudzi kuno tikuvutika ndi njalaaa!!! Naweso amene ukunena kut akapezeka munthu akunena zot mkuluyiii akudwala amangidwawe ndiwe mbuzi ya munthu wava galu wachabechabe tangooona mzipatala mankhwala mulibe,, bwanji mukadwala mumathawila zipatala zoodula?? Bwanji mumakana kudwazikidwa mdziko lanu? mbuzi za atsogoleli tatopa nanu
Wea is our beautiful malawi i know. Bola bingu he was wiser than this. U guys u r busy dancing for him wat for? Mark my words we r in crisis zimbwabwe better.
Nothing to say!
Ndamva
Ndemukuti amuthalika akugwila ntchito zina kwamereka ife tidziva zopusazo chabwino ngati ali moyo auyambileso ulendo abwele kaye kuno ameneyo adzaone swichi yama getsi apa simwati ali moyo koma ine chomwe ndiku ona ine kunja kuno ndiku ndende palibe kusiyana sindinga siye kufalitsa uthenga kwa ntundu wa amalawi kuti muthalika wamwalila tili kundende kale pano bolani ali ku sero palibe kusiyana ndife kunjakuno kwavuta bola timangidwe tizikadya nawo za msokho zo basi tinafa kale pano kumalimbana ndi kupita ku school kumati tidzapindula nayo fees inandi pweteka kukweza kweza ndinakupililani pano ndikungo shala kumalingalila kuti school fees yanga ndikana ngo yambila ka geni or kogulitsa makala ndibwezi pano nditaiphula ndezomwe amapanga gönthi ameneyu sindi mafila ndikubwelezaso kuti amuthalika afa mukandi funa mundipeza ndimakhala kwa tambalale
Sizikugwilizana…Bwanj osamanga mbava za cashgate, opha Robert chasowa ndi matafare, Chilungamo chidziwike ife ndiye tiyankhula mosalekeza…Mutimanga pa chilungamo
Apa ndichimodzi modzi kuti dziko lilibe president likudziimila lokha.
Wamwalira nanga alikuti poti mbudzi simayenda ndi m,busa
Kkkkkk sindimafuna koma mmmmmmm ndiseka ndithu
kkkkkkk apite alondole achimwene wake basi
Guys tisataye nthawi ndi mphekeseraxi tiyeni tipange zathu cz kunalembedwa kut aliyense adzafa kulibe wamuyaya ngati a President amwalira monga mukunenera kwao kwatha kwatsara kwa inu ndi ine.
Aaasaaaaa za chamba eti. Boma ndilimene likupangisa anthu kunena zaboza chifukwa silikulongosola chifukwa chomwe a president athu achedwela kubwela , ndiye timanga aboma omwewo sadziwa ntchito yawo ya information
But what i know is that there is no secret under the sun! may GOD bless malawi.
There is no smoke without a fire????????????
Amangilakuti?
Mutharika is still alive ndinakumana naye zulo mu supermarket akukagula tomato and he tald me that he ll go back to Nyasaland when his life is finished. Umu ndimmene timakhalira umoyo waziko lapansi so lets us look up and our tears mst go inside our stomache. An ask God to gv us another gud leader. My his soul rest in peace ngat mwamwaliraT_T
Please a minster imfa ndi yowawa we don’t want to lose peter again tanenani chilungamo ngati akudwala tili nda a zitumiki ambiri amupempherere please kodi mumakonda kubisa zinthu bwanji
Atsaaa amangindwa??? Tell us which is which,, to avoid these rumours
Akufuna atibweretsere peter wa surgery
DPP WOOYEEEEE!!!! IFE ZII ZII ZII
Vuto nd chan? Czotheka ,alikut?
there is, there is/ kalipo kalipo. they want to walk us mathematics/ akufuna kutiyenda masamu,,
Kusiya umphawi wa mudziko lake kupita kwaeni ndizina lake Pita wapitadi kaya ondimanga andimange ndatopanazo zimene akupanga ma president a m’malawi hahahahaha mnawaaaaaaaaa
mmalawi amafuna kudziwa zoona basi osati zamikuluwikozo kodi ngati simukumuza chilungamo mmalawi nde mumuza ndani?Chabwino tamva ndikukhulupilila kuti amalawi sakambanso zimenezo.
Mukulephera kukhonza vuto lamagetsi koma kumanga nde namba 1. Bola akanamwalira mwina magetsi alibwino dziko muno. Nditengeni
democracy ndichani
TINAVOTERA NYALI kuleka zomzngana akati ufulu ndichani maiko ambiri amanyoza mutsogoleri wawo koma samangidwa tiope mpaka liti zinthu zavuta kumuzi timangeni ngati tili muchipani chimozi
Ndikuganiza kuti mwina a President ali patchuthi. koma aboma achita dala kusalengeza chifukwa choopa kuti anthu anganene kuti nkuluyu sanayera kukhala patchuthi kamba kamavuto omwe ali mdziko muno. Baibulo limati zinsinsi nza Yehova,koma Zobvumbuluka Zinanatsidwa Kwa Ana A Anthu. Tiyeni tidekhe.zeni zeni zidziwika.
Matenda bisani maliro timva
timangeni apolice koma chilungamo chiziwika posachedwa coz if he iz in gud emotion y he iz failing 2 come back home y ?
Mukalimbane ndi Mmalawi nzanu zoona,osakamanga akutenga Nyanja ngati mphanvu zachuluka bwaah?
kodi muthalikayo ngwambeu mukuwpsyezanaye amalawiyu? wakufa saopa kuwola tiuzeni zowona tisamachite kimvela mayiko anzathu zaprezdenti wathuyo
Uchita bwino ufe . Mwayesa ufumu womangolandilana pamtundu basi. Uziwona sudati. Mafuta,magesi kumango nkhalila kuvuta basi ndalama mutaba agalu inu.
kulankhula mwantudzu kumeneko tikuonelani
Shatup zako manga ineee! Peter Muthalika wamwalira maliro abwera mawa pandege
Bisani matenda maliro okha tidzamva abale
Zausilu olo atafa ndibenaye ntchito ino abwele mwana wapoli osasamba azandimange
NZIMU WAKE SIUNGAUSE MU MTENDERE CHIFUKWA MUKUBISA CHILUNGAMO. MUMANGE INEYO. NKHAWA NDINAPACHIKA MU MTENGO WAKANKHANDE
Nde muwonjenzere ndende nanga tizakwanamo
WAMWALILA BASI PALIBE KUSINTHA
kusowa Kwa ntchito,kuzimazima Kwa magetsi,kuvuta Kwa madzi plus njala ukaidi upose apa lne nde Bola munditengere konko basi
Zikachitika palibe kubisa
muzikamanga azigogo anu’zauchisilu
bisani koma timva
INE BWANJI NDIKHALE WOYAMBA KOZ NDATOPA NDI NTCHITO
MZIMU WAKE UWUSE NDI KAMTENDELE
Big wo akanabwelako kuti zokamba kamba zithe tizimva nkhani yakufa si yabho by akometsa smart
wafa wafa ngt akhal oyamba iyey?
Akabwela alembe lipot kkkkk ifetikaniomba ku vep opanda chifukwa timalemba naye alembe
kkkkkkk tifuna lipoti akabwela kkkk
Ngati wamwaliladi kumalilonso sitizabwelako.
Let’s see ngati alimoyo that’s all.
Mpaka kumangidwa ndie zafikapotu???….
Peter munthali no more RIP
Ause mumtendere
Kodi mesa mumafalitsa zoti wamwalira ndinu nomwe!!? Pamsanapanu!!
Pulezident wa dziko la Malawi polofesa Afa Petulo Muntharika wasowa ena akuti wammwalira malingana ndi ma ripoti.
Ndemutimanga ambiritu
Tikalowa, koma nayenso Malipilo amwezi uno asalandile.
What about those pple who are in foregn countrys and they are busy saying that president peter dash dash is deid are u going to follow them wea ever they are to arest them? I think is jst the waste of tym to deal with this GOD BLESS MALAWI
Kkkkk ndimangidwe ineyo=pitala wamwalira
Ukalembanso uzasowa kkkkk koma ndye tilinso must nthawi yodya madeya atiligu yomwe ijatu.muuzeni ayankhule yekha life timber kkkkk.DPP izi sidzachilendo kubisa matenda kapena maliro tiyeni tikhale mutiuza nokha
Its Not Our Fault But Goverments Fault By Not Explaining Well What Our President Is Still Doing In America Weeks After The UN General Assembly And I Appeal To The Goverment To Give A Reasonable Explanation To End This Saga
Ife tamvera kwainu nde chonde siyani nkhaniyo ngati mwapangana ndiomanga mumvekere ndikupezelani owamanga pepani ife ndale stinapangepo muzipanga ndi andale anzanu
Zeni zeni ziziwika
kod asapite kopuma?
Lol keng jwallo
akumunamizila nzakoyo?
Kodi afadi akuluwa?
Zaziiiii amangidwe chifukwa
Kod presidentiyoi nd wathu tinamuvoteranso tokha osatiopsyeza ayi
Oyamba kumangidwa ndinu ngati wamwaliladi
ife sangatimange
Zazii alikuti nanga tiuzeni zoona
nthawi yathu yovina abwana ndiulendo mumabottlestore mose be ready with our tokenz anga a2thousand ali mthumba
Mutharika wamwalila gyz
Amangidwe ndipresedent-yo nanga akupangisa amalawi kupalamula,,akutaniko iye ku ntchire,,zopalana mkamwa basi
NDAKATULO… = Chilungamo : ………………….
Koma guys…….. Kkkk…. Kkkk
Kodi Madam President Ali Konko?
Funso alikuti mwenzi ndi masiku osamva mau tangomva maward..
let me be the first to person to be arrested so that enawo atengerepo phunziro!!! apo biiii ndikuti “”#bwampini_wamwalira
Koma mumathamangila kumanga kaya mumapindula chani koma mawa muzafuna voti kwaomangidwayo zopusa olo chitafa chilibe phindu pa dziko pano iya sitiopa kanthu apite pitalayo basi
Tiuzen zoon
kkkkk akuti ku america sikufera president
Ok tamva mutimanga koma zikangokhala choncho a Ndau tikumangani ndife mudziwanso. Ndinaiwala, muwauze a pulezident atiyankhule via skype ngati ali bo.
Rest in peace mutharika
esh tidzaza kundendeko,,,timuone pa mbc tv or alankhuleko pa radio ngat alimoyo,,,kaya mutimange sadzukabe ameneyo ngat wamwaliladi,,
Nafeso tikumangani a Boma mukubisa maliro kwa America.
Zikuveka kuti wayamba kuphuzitsa ku university of indiana
timangen man we do care magetsi akuvuta zusiyana pat kundende ndi kunjakuno
Inuyo munayenela kukhala oyamba kumangidwa coz ine sindimaziwa ndamva kwa inu a malawi 24 nde mukamati amangidwa ndikudabwa nanu kapena muli ku ndende komko?
Hahahaha, mpaka kumangana zomwez? Ndiye kt something is happened to him,bwanji osamakamanga mbava zkuwononga tsiku n tsikuz? Criminals are every where due to poor security but you’re busy threatening pple for personal issue lyk dis.komatu chouluka chdzatela zibisana there is no secret under de world coz enaso analipo ankabisa koma znaululukabe.
Mkut Sanamwalile Ndy Alikut Tikuvuka Ndalama Iyezikadya Kumfusa Akut Alibe Problem Ndy Mkafuna Kumanga Timangani Tose Kuphatiki ZODAK Ogo!! Olakwa Ife Hahahaha..
kkkkkkkkk a boma ine musandimange nawo sindinenanso, apapa ndidzinena za president wa FAM a walter nyamilandu kkkkkk
bwerani mudzandimange ine ku south Africa kuno.. poti inexo ndauzako anthu angapo
Truth shall set us free . then, tell us what take him so long and when z he coming .we are tired of here says
Kod mesa faz imati anthu akamakunena kut wamwalira koma uli moyo amakhala kut akukupatsa moyo wautali???
You Stupid MBC, u are fond of parading stupid dpp Jumbe on ur TV. Can u parade ur Muthalika for all malawians to prove that he is alive and kicking? Why are you stupid quiet instead parading stupid propagandas? MBC you are the most stupid shameful station in Africa. Nenani za Muthalika timve kuti tikhale okhutira kuti iye ali moyo…ndinu vopusa zedi inu kutaya nthawi kumaulutsa zopusa basi, rubbish zanu basi .
U can write that again and again….and again, they are tryng to play monkey tricks but it won’t take them anywhere….
All what I can say, I don’t evin fil sory for Peter, he’s very rud to people he jst talk they way he want, he don’t watch he’s spich wen he talk to people, he think tht he’s heven but not at all, nd I pry tht he must die if he’s not die, if he’s already past away that’s gud, nd I say thanks god for doin all this job……..
wamwarira wamwarira basi bwanji sakuyankha ngati alimoyo nde mumanga angati?
Tamuimbilani 4n ndipo muisiye pa hands free timve nao ife akumudzife. Koma ikhale radio 1
Ngati walithawa atiuze tidziwe chochita,ngati wamwalira, awusemu mtendele. Koma ngati akusewela azibwela mavuto anayamba yekha sitinamutume.
Mmm!! Zovuta zed,
palibe zomanganapo apa iya
Ndakozeka kumangidwa ineyo ngati ndatukwana muthu samafa adzikafa mandera uyuso ndani
Anamwalira ameneyo yemwe mukumuonayo ndi ndondochaa
Ara antimange zautsilu eti anayamba ndiyeyo kumwalira rest in peace
mangeniso nyamata uyuuu…………..
mangeniso nyamata uyuuu…………..
Nde apange changutu,coz kankhanika nde lafala heavy….
Nde apange changutu,coz kankhanika nde lafala heavy….
Amangidwa chifukwa chani? Hahahahaha, ine sindikuopa
Amangidwa chifukwa chani? Hahahahaha, ine sindikuopa
Aaaaaa zautsilu eetiii ndani angamasekerera zoputsaziii iyaaaa!!!!!
Aaaaaa zautsilu eetiii ndani angamasekerera zoputsaziii iyaaaa!!!!!
Kulibe zomangidwa RlP basi ndalama kubisa ngati chani .
Kulibe zomangidwa RlP basi ndalama kubisa ngati chani .
ok ine ndanena kuti akudwala. dzandimangeni. kulibetu wamuyaya
ok ine ndanena kuti akudwala. dzandimangeni. kulibetu wamuyaya
mmuwuze omangayo amange kaye ameke ife sitiopa zimenezo ayi koma tikufufa chilungamo basi
mmuwuze omangayo amange kaye ameke ife sitiopa zimenezo ayi koma tikufufa chilungamo basi
mukuti mukunamiza ana? ndi kukambirana kotani kosadziwa international media iliyonse? zopusa basi
mukuti mukunamiza ana? ndi kukambirana kotani kosadziwa international media iliyonse? zopusa basi
Mwauzeso abwele ku south Africa kuno azanditenge kuti andimange ine iyeyo wamwaliladi coz president akamwalila salengeza sikulomwero tikuziwa kuti mukutibisa
Mwauzeso abwele ku south Africa kuno azanditenge kuti andimange ine iyeyo wamwaliladi coz president akamwalila salengeza sikulomwero tikuziwa kuti mukutibisa
Mwat chani?
Mwat chani?
Timangen..we don’t care..hahahah..anyone who fears death is a coward..
Timangen..we don’t care..hahahah..anyone who fears death is a coward..
Ndimaona ngat muzinena kuti m’gaiwa wasika m’tengotu,ndye mukundiuza kuti mundimanga???? kkkkkkkkk zachibwana izi,ndipaseni machine gun buuu!!!! ndakushutani nonse
Ndimaona ngat muzinena kuti m’gaiwa wasika m’tengotu,ndye mukundiuza kuti mundimanga???? kkkkkkkkk zachibwana izi,ndipaseni machine gun buuu!!!! ndakushutani nonse
Atimangetu
Atimangetu
Anthu anji omasangalala ndi nkhani zosafunilana zabwino Malawi watan sick? Mmesa mumati ndinu oopa mulungu so why this?
Anthu anji omasangalala ndi nkhani zosafunilana zabwino Malawi watan sick? Mmesa mumati ndinu oopa mulungu so why this?
ngat sakudwala muuzen mawa azibwela tikumufuna zomanga izo ayi
ngat sakudwala muuzen mawa azibwela tikumufuna zomanga izo ayi
Sopano ngati sanafe kapena sakudwala nanga ali kuti nanga akutani? Tiziti mwina wathawa? Ziko lamukulira? Kapena kiddinaped ? Malawi ali pa mavuto uyu, anthu akuthawira mmayiko ena naye muthalika waionera patali wabanduka, anyway not get well soon or rest in peace
Sopano ngati sanafe kapena sakudwala nanga ali kuti nanga akutani? Tiziti mwina wathawa? Ziko lamukulira? Kapena kiddinaped ? Malawi ali pa mavuto uyu, anthu akuthawira mmayiko ena naye muthalika waionera patali wabanduka, anyway not get well soon or rest in peace
NGATI WAMWALILA WAMWALIRA BASI
NGATI WAMWALILA WAMWALIRA BASI
You’re Such An Idiot….And You Don’t Get It Do You??..Let Me Put It This Way To You Mr Editor….Its You Who Has Just Written That He Is Dead So What Do You Think Of Reactions On This!!
You’re Such An Idiot….And You Don’t Get It Do You??..Let Me Put It This Way To You Mr Editor….Its You Who Has Just Written That He Is Dead So What Do You Think Of Reactions On This!!
Awaso ngati chilipo chimene akuchita iweso walemba pasi pa mtima wako ukudziwa komaso ukayambe kumanga agogo ako
no oppression let the truth out ,mungotiuza zomwe akuchita kwa American
Wachamba amene akunena kuti amangidweyo
Information minister you are fired. Hw can you alow pipo to spread bad news about our president, and what we know is he is in america, overstayed without a reason all leaders are back to their countries. Just come clean to stop these bad news . We need answers with all respect it is costing the country billion.
ahahahaha truth pains he is really dead ndekuti.
Yetsani kumangapo m’modzi muone anthu oputsa inu
Aaaaaa ndie zachambatu iwe ukubisa malirowo
Namwahuno !?wakuchitachi?
Oyenera kumangidwa ndi iye amene wasiya ana ake panjala .ndikupita kudziko layeni ndikumakadya kumeneko zakasinthasitha pamene ana akefe kuno tikumwa denje ndi therere la chewe . Tsono mutimangilanji poti ife zomwe tikufuna ndizoti iye abwere alimoyo osakhala ntembo ai .
Nangano chikuvuta ndichani kuti munene chilungamo .koma kuti opsyeza kuti mutimanga .ok let me say hello to de president .and ask him lyk this ; “Mr president, when a u coming back from U S A ?and when will u tell us de truth about your life Mr president? Could u plz tell me exactly what u are doing da in de foreign country Mr president ?
Do u really think abt your nationality Mr president?
Or do u know hw mch pple missing u in your country ?
I hope he will ans me .
tiuzeni kumene alitu nanga
amalawi 24 kod nkhani zanu mmazitenga kuti ?
Koma kumangako mukanakhalakut mumamanga anthu olakwa bwezi mbiliyanu ilyabwino koma Ah mukulimbana ndine mukusya oba ma million, mpamene mumadziwikilakuipakwanu pamenepo!
Sibwino koma ukundi kumuderera tsogoreri tiyeni timupatse uremu wapadera.
GUYZ AMUYAKHULITSE NGATI ALIMOYO
Ngati sakubwera ndekuti akudwara or watisiya.. Ngati ali ku holiday tiuzeni tiziwe mkutibisa chifukwa chani mesa tinamsankha ndife nde tikuyenera kuuzidwa kuti chikuchitika ndichani
371 starting Thursday
Malipiro awanthu am’boma ndi misonkho yanthu ife tikajomba kuntchito amatidula malipilo peter naye adulidwe salar wajomba kwambili ngati akudwala azaonese kufuko lamalawi mapepala aku chipatala mukhale masikuso
Zao izo azibwera
Kkkkkkkkkk ok
zauchitsiru bac kod mukutitenga ngt ayani?? tangoxunga ulemu chabe km tili ndmkwiyo… wapolice yo naexo chtsiru ayerekeze kumang mun2 muone,,, kod akuganiz ngt tikuopa eti?? ngat wamwalira bac ifexo tathokoza kt zatelo ngt akudwala tingoti aptilize kudwalako kaya amwalira tilbe nazo,,, ucitsiru wamun2 wamkulukulu bwnj?? mukanene zenizen kt boma ili latikanika,,, km zoti tikhoz kumaopsezana cfkwa chaucitsiru wa pitala izo ndie iwalan
Nonsense. If his no dead tell him to speak to the public we are waiting to hear his words
Then where is he? Tell us
RIP prof if it is true
Okay ndamva
Ndiye tigwirizane, mudzatitulutsa akamwaliradi? Sinanga tidzakhala kuti timanena zoona.Kkkkkk!
May his soul rest in peace…#tikumane padedzapa timangane basi
kodi zikuteloso?
Timangeni koma ngati wafadi nde mudzatitulutsa Eti?
Peter is dead already
Ndiye tikubweleranso thawi ya Kamuzu2 yomawopa kulakhula za presdent akangokumva a youth umakhaula….pliz government its 2016 we can say about the presdent whatever we want.nt long ago primary kids called him bwampini and no1 was arrested..if the presdent is stil alive let him come back home and prove this rumours wrong.let him come nw and do what he is paid 4 than lavishing tax payers money 4 nothing.thats if he is alive bt if he is died we wil bury him ndata is waiting……..
Tsono Mubisira Anamalirafe,ngati Afadi Mudzalira Nokha?
You pple,if the guy is dead,is this the protocol?being the first citizen let’s respect him.he shall come,stop nonsense,if he is gone you fill he will be buried where he is?
Nanuso a media mukalengeza kt Muthalika wamwalila tikumangani,sinankha mukufuna zomanganaaaaaaaaaaaa
Ngati Ali Ku America komkuno umuuze andiflasheko potipa ndimpasile zinthu…..
Shhhiah!!! That’s a Democratic Malawi in 2016;enforcing colonial laws where £1000(pounds) is the fine. I need Bakili to explain what democracy he claims to have championed when the laws are so archaic.Shame! We are still in transition huh!
Kkkkk bodza lochititsa nseru kodi eti. Ha ha ha ha ha ha ha ha
Now what if its true are you telling the nation to summon the Malawi police? This is a lame decision made by someone in command. What if someone is arrested and that exactly the death follows and the postmortem showing his death before the suspects mouth, will the police continue keeping such suspect in custody or they will implicate him or her that he is being prosecuted for unlawfully disclosing the death of the head of state in public without proper authorisation to do so? My head is aching now…..Government must come open and civic educate us first before claiming that it will arrest our laymen who don’t understand the consequences of such grievous act kaya mumati dismenour kaya za law simbali yanga, bola mwamva.
Uzingomanga anthu chifukwa chiyani mr president?
Tiuzen Zoona
apangidwe interview pa mbc kut tikhulupirire alibhobho sizomanganazo apa shupit
If the minister is saying the truth then i wish my presdent gd healthy,,,,,bt if he is lying adziwe kuti akuphwanya malamulo ndi iyeyo ponamizila munthu omwalira kuti ali moyo,,,bt i blv my presdent is alive and relaxing somewhere.
Minus ndende…for me what we are doing is inhuman…lilime lilinayo mphamvu yolenga moyo ndi imfa..tikupeputsiranji umunthu wathu a Malawi
ngat ndikumanga ndiye muyambire ine kumanga sitisiya kufalitsa uthenga oti peter wafa unless boma litiuze zoona pachifukwa chimene iye akukhala kumeneko-arrest me now!!!wafa basi mtembowo ungobwera tidzayike basi mpaka uwolera komkotu
Nde mumanga dziko lose eetu
ngat ndikumanga ndiye muyambire ine kumanga sitisiya kufalitsa uthenga oti peter wafa unless boma litiuze zoona pachifukwa chimene iye akukhala kumeneko-arrest me now!!!wafa basi mtembowo ungobwera tidzayike basi
Ndipo ine ndikunenadi kuti wa mwalila abwele poyela atiwuze ife ndipo tinena kuti RIP bwelani mudzandimange kuno mtundu wa nkhanza uwu iyaaaaa
Bitsani matenda koma maliro tizamva!!
Kkkkkk amangidwe makape winaso apa akundifusa kt kodi anse phata mutalicka sogoleli watu kumalawi wamwali lila ndamuyanga kt ayambe asogola kaye agogo ako yooo comment
President wanga okondeka,wapamtima adakali moyo komanso wamphamvu,iwe ukumafalitsa nkhani nkhani zako zopusa ndizopanda nzeru,ukhaula chifukwa very soon u.w’ll see him coming back 4rom america ndipomwe uzazindikire kuti “mulungu si jemusi”Mr president tikukufunirani zabwino,umoyo wangwiro mpaka pomwe muzabwere,tilipambuyo panu mpaka 2024 woo!!asakufunayo akakolope lake Malawi.
Y Lord??Why have you let yo pipo tu suffa fo so long now Yaweh onetsani ukulu wanuuuuu
ofunika Kumwa uwiri Kaye nkumawerenga vis post ,lest in pc Mr presdent ngati ndizoona anthu awone zina,munayesesa kuba kumbali yanu koma mulungu wakubani ngati cashgate kkkkkk
Amshona kuwupalanga mwaaaaano kkkkkkkkkk!
Dont play with fire u dpp minester of enformation by saying head of state is doing ather duties of bannefiting the malawi national while he is sick or daed as how the rumars is spead all over that he is admited or dead .the vice presedant and all ministers u know the trueth dont put the cut in the box guys bcse smoke does not shute up without fire.if the trueth cames out that he is dead or admited people will suplay doom on u for telling lies to them worch out .from the office of firgatud-dawah durban south africa wrote these massage:peter muthalika the president of republic of malawi is dead. This has been confirmed some minutes ago by hospital authority in us.we begg all malawians to stay calm as we pass through this time.where these ngo gate these rumar
Oyamba kufa ndiiyeyo kodi?
Wathawa munthu wamkulu amaona ngati ndimasewera kulamulira dziko wachimina!!!
ndimuuza bushiri akusowese
Zam’maboma RADIO 1 & 2, zikachitika mvera kwa ife ZODIAK, street talk CAPITAL FM, thumba la tambe amamasula nd tambe yemwe TIMES RADIO, KKKKKKKKKKKKKKKKKKKKIYO, tell me whch radio should i be listening to?
nde auzeni anthu zoona zake
ufa osadwalatu
Nde ndende zizadzat
kuyambila amene ali k u America yo ndi amene akunena zomangayo Kunalibe mmene azawo amavutika ndi demokalese azingothokoza kuti ndife amasiye adangotola nkhani mwabweletsa nokha kubisa komwe kuli a pulesident wa Malawi abwere adzayankhe mavuto ali munowa paja ndi ophuzila bwino muno mulibeso ndiye timavutoti angowelenga ma book ife tione kusintha iya
R I P APM
H z not dead,ndi macheza naye pa watsapp dzulo madzulo
kodi munthu kunana kuti wakuti wamwalila ndi mulandu kani nde mutiuze kuti lamulo limene lili pa # yanji ife mkuyamba kumva
Everyone is important in this world so please don’t let Mr President to go faster than he was born because aliyese alindizochita zake pano paziko lapansi.
Nde Akuwopsesa Ndani Ndiye Kuti Wamwaliladitu Ayelekeze Kumanga Munthu Muno Ngati Sanafe Ndidzachita Kupha Ndekha Wapita Kumeneko Ndi Ndalama Zanthu Ife Ndikumavutika Kusowa Magetsi Kusowa Madzi Nde Ndikumati Atimaga Sindingawope Amagidwe Ndiyeyo Cause Watibela Ndalama Wakapatsa Ana Ake Ku USA Mumuwuze Ayambile Ine Kumangako Akandipeze Ku chisapo 2 Akawone Zimene Ndimanta.
Stupid umuuze
Amangidwa?,kapena ama-ngidwa?(has been arrested or they’ll arrest?
Kkkkk ineso ndili pano
Zopusa inu zimenezo,every citizen of a republic of malawi has a right to know,
kkkkkkkkkk iiiiii mbudzi ndi mbuzi basi kkkkkkkk inu muziwe ndinu ndani aaaa wosamangodya gaiwawu bwanji? olo mutalimbikila angakuuzeni chani inu aaa akapolo adziko
awuze asatiopyeze
koma apa magayez ndiye mukuthoka ngamutu kkkkk
oh boy
zviri kunzii bambo
May his soul rest in peace ………iyaaaaaaa amange basi
Wafabe
Kkkkkkkkk zobvuta kwambiri
Leonard Dzanja mumangidwa nazo izi ndithu enanu ndinu akapolo adziko ngati ine pano aboma tiuzeni zoona bwana alikuti? ngati akumva atiyakhule ife
#Muthalika is very useless man he can to left #Malawi without #Water #Food #Electricity chonsecho iyeyo wathawitsa masaka andalama xomwe wabela a Malawi ndipo tikupempha wadzisomoyo kuti #Pitala_Namathanyula afe ndithu Kaya ndi malungo Kaya ndi Nuclear n asadzawerenso kuno
Fuso labwino kwabax
Zachamba eti pali be omangidwa apa
Koma ndiye amanga ambili
Amangidwe?
Ayenera amangidwe kumene!AMalawi tidakhala bwanji sitimafunira mtsogoleri wathu zabwino?Umenewu ndi moyo wauchikape.
Nenan moti dziko liziwe,nanga alikut
Zoona nziti nanga?
Or atamwalira ndilibe naye ntchito kwakwananda ngati ameneyu mixew
if it is true that he is dead may his soul rest in peace
Ali kuti nanga msonkhano unatha,
Kkkkk All eyes on screen gents …We cud watch 1 of the most astonishin’ news of all tym!
yesu anafera ife pamtanda,km awa afa kamba kazocita zawo,musatimange remember kt anthu amafa,weath u lyk or not bt u born to die
Zachamba eti ukayambe wamanga mai ako musatiopyzeze dzikoli ndilathu
Musawaopseze anthu ngati wamwalila wamwalila basi,anamwalila Yesu ndiye Muthalika ndi ndani kuti asafe?Bisani koma tidzamva basi Chilima komzeka.
When Bingu was dead they took his remains to SA spending and looting money in the capital hill then they announced that he is dead.Now with this bastad haaaaa poti Ali ndi American citizenship mwina maliro ndioika komweko.If he is not dead then he is full filling the American citizenship laws where by anyone with green card need to stay in America at cetain period of time otherwise you may lose the card.
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
Kkkkkkkkk zaziiiiii nde mumangiretu ndende ina poti okambafe tachulukitsa sitikakwaniramo…nanga ingonenani akuthawa chani mu dziko lake azake anabwerako jale kumeneko.chilichose chobisika pasi pathambo chidzaululika
Zoonadi Mr #Masia Lungu Muthalika akuyenera kudzalandila Chibalo , osati Chifukwa ndi msogoleri nde azipanga zofuna zache mayazi ! Asaopseze a2 kuti amangidwa 4What ? No !!!! Palibe mu2 amene amamangidwa otsalakwa umenewo ndi mwikho !
za chamba
Wafa wafa amangidwe nda yesu ngati anafa pitalayo ndindani
Ayende being tidzakaobana.komanso usi sufuka popanda moto wamwalira wamwalira basi kumangananso kwachani zanzii basi
Wamwalila basi,nothing for hidding ,Chisofa basi chituluke nyumbamo ampingo alowe ndi nyimbo yawo 371
Hhhh ayende nyatswa chilima m:bwalo mwina dziko la2li ndalama ikhalako yambabvu
Kodi aboma mumabisa chan? Bale wake zinalinso chocho mumkabisa atamfa uyunso ngat wafa sizot mukabisa adzuka kwa akufa!
Opusa inu,ngati mukubisira dara kuti Peter wamwalira and ife tikuwerenga zinkhani zoti a president amwalira mukuti tisawadziwise abale ndi anansi kuti adzikonzekera kukakumba manda ku ndata farm? ndipo ngati mukuophsyeza kumanga onse amithenga,mukwanitsa? timangen……tu
What’s is all about you know this one is the president of Malawi. Just tell us the true. Why you are hiding same thing. But what you can know is God is not hiding
Kkkkkkkkkkkk guyz
Shupt Guy…xopano Mexa Akudwala mwakayakaya Mbuz imeney bwanji
Ayambire iweyo poti ndiamene udandiuza kuti abwana atisiya
Patsogolo Ndi DPP Patsogolo Ndi Chitukuko Dr Peter Munthalika Kasupe Wa Chitukuko!!!
mmmmm koma nde mutivuta yoh zoona koma or atati ndendezo mudamangila osalakwa zoona hhhhhhh zukachitika tiziva n tikakumana komweko amen amen
Mundiike nawo pa list yo pliz kkkkk
Coment stili loading……
The chances u take and the mistake you make my God is writing on the wall
Mungomuchedwetsa chilima apa aaaaa tikhaleko nditsogoleri owoneka bwino ndithu..
nde ngati wamwalira muzizawauza anthu omwe mukuwanamizawo kuti tsegulani mawailesi kumvera mwambo wa maliro? palibe azatsegule wailesi or TVM apa ndi mabodza anuwo
Kodi onena kuti Mutharika wamwalira, ndi anthu aja adaba Ndalama za boma aja, oyenera kumangidwa ndani?
Fuso labwinobwanji, ndchifukwachani amakonda kuweluza obankhuku oba galimoto ayi??
palibe wina adzakakamize wina kufa pokha pokha mwini moyo ndi kupuma mukupumako atalamula kuti mpweya wake uthe .icho ndi chigamulo cha iye mwini .zofuna za inu ndi ine .sizomwe iye akufuna .
Nanga Asilikariwa akupanga chani ku ndata farm pakuopsa kudusa pandata amene wadusapo andivomeleza….kaya shame
kaya zanu izooooo ife tikadali ana
Is one of bad law onse anthu would not wish him will. Komaxo amalawi tanyanya kodi akafa ife tipinduranj. No SENSE. BWANJI osamalimbana ndi mavuto atiwilikiza kut achepeko
aaa musaopyedze anthu nangano alikuti mpaka pano kumweko ku america
osamanga cashgate members bwanji??
Nde alikut ndipo akutani? Mumanga bwanji munthu akufuna kuziwa komwe kuli m’tsogoleri amene adamuvotera yekha?
umunthu kumalawi kulipe pali zaboza kukamwa mbe ndakhulupilila bodza limapitadi patali koma akukamba bozalo agona ndinjala.
Bwanji mkulephera ku tiuza choona chenecheni
Wafa wafa basi watinzunza galu ameneyi munchele masende ake
Abwere poyera timuone ngati sana mwarile. Aboma fikani poyera muudze mtundu wamalawi zoona zake osati mubise ai.
vauxeleza umangenjan
Then muwuzen azibwera ife timuone aaaa
ngati akudwala ndiye n’kolakwika anthu ake kudziwa ?
You should be the first one to be arrested
iwewakutuma ndani kutiwunenezimenezi iweyo ndiwokutuma nose ndinuzitsiru pamodzi nditsogoleli wanuyo shatapu
We Malawias Chilungamo Kuvuta Apm-wa Angobwera Pakanema Iliyonse Ndikuwuwuza Mtundu Wamalaw Kt Ine Sindikudwala Bas Lumour Itha Zikatelo
Zamanyazi Akubisa Chilingamo Mune Nokha
mwina amawaphikira anzake nde asala akumaliza zosara. Tiziti iye ngwaphindu kwambiri azake onse ochita bwino anabwerera ndiye kuti iye akusuka mbale kkkkk
Pajatu anamanga mudzi onse ku Thyolo posachedwapa. Azolowera. Nde from Nsanje to Chitipa, Mchinji to Likoma tonsefe tikakhale kundende? Ufa wake inu a Maliseni mwaupedza kale?
I thought onse amene anapita ku America limodzi ndi Peter anabwerako? nde what is he doing alone? tiuzen zoona apapa
Kumanga anthu pachifukwa chani, khalidwe komweko lo ophyedzana basi, musintha liti, nkhanza mpaka mudzalowanazo m’manda!!!!!
Ngakhale Mukubisa Mukunya Nanga Sikupopeza kutikufusa Ndiye Tikukhumba Kamalilo Ko Kapena Matendawo Ayi
Kodi APM wasanduka president waku america??
Ha!ha!ha!ha!k!kkkkkk!ho!ho!ho kwangali comment
Kikkkkkkk mpaka ndende tufuna tingoziwa zoona zake
He must follow his brother, we don’t want him back,we are tired with his nonsense
No comment
Umanga angati ?????eni kuvota akufuna kuziwa choonadi mutipusisa mpaka liti???
nanga poti inu mwanena akumangani?
Mundibweretsere mtsogoleri wanga
Rip(return If Possible)
Tioneseni Pa #MBC Ngat Alimoyo Ndichomwe Tikufuna Ife Amalawi.Zikatelo Tisiya Kunena Kuti Our Preseden He’s Died.Vats We Want Bas
Kulibe kumangana ngati wamwalila uwuzeni thundu wamalawi kuti bambo wathu watisiya ngati ali moyo abwele pa MBC TV titsimikize chombisila ndichian dziko ndiwathu ngati mwapsa mtima awuzene apolice adzandimange ine ndili BT pa mbayani pompa pafupi ndi kambula police
hahaha..nde ingotimangani bas..Mdala paden sikuoneka tisafunse?Atiyankhule usiku uno…chilipochilipo bas..
Anthu openga inu et peter akulimbikila kupuma kut asafe akabwela ndithu munjatiwa koma akachita ulesi ndikupuma aduwa 2019 wooooooo
Matchaya bwa?
Tapitani muone pa BBC News
tiuzeni chilungamo. bambo ndi anthu south africa yalengeza kuti akudwala. kodi bwanji mukutibisa anthu inu
That’s Malawi politics
The fact that he’s dead could definitely be true bcoz under his leadership Malawi has never been the same as before! He robbed and cheated the poor people all the time. Thank you God for solving this problem out for us!!
Ng’ooo
zopusa bas,,pali chfukwa chomangla munthu apa?.ngat mwakhuta pitan ku toilet .stupid
Ok tamva ziko lopanda khalidwe ili kumanga, umanga ndani? Umange eni dziko eni ake amene akumakupangisani kuti ku U S A aziwe kuti kumalawi kuli presedent ndiye mumange ovota, ndiye pali nzeru apo? Ndiye kunyela pambale yodyela ndapita ine mwana wapa Nyika Republic.
Pakati pa Dziko la America ndi Dziko la Malawi loyenera kugwililidwa ndi ntchito za Boma ndiliti ? Tsopano A Muthalika akuthandiza Dziko la eini kusiya lawo ? Ma President onse adabwelera mumakwao tsopano Iwo a Muthalikawo ndi ofunika motani mu dziko la America ? Ngati anthu akutchukitsa zoti a Mr President Peter akudwala kapena amwalira izo azipangitsa okha kamba kokhalitsa mdziko la America . Palibe zomangitsana waba ndani kapena walakwa ndani ? Angobwerako azipitiliza ntchito za Boma basi sizoopsezana mwa uchitsiru apa ndiponso Kkkkk kkkkkkkkkk Muthalikayo akabwerako agwire chibalo kamba kojomba Ku ntchito iya nanga tiname hahahaha .
chibalo chake akafukure mtsinje washire tikufuna magetsi ife asa kkkkkkkkk
kkkkkkkkkkkkkiest i rest my case
Mr? Address him accordingly plz…
good reasoning man. and muthalika has to be punished for not being in office without proper and relevant excuse to his bosses who are the malawians kkkkk
May his soul rest in peace kkkkk …..asaaaaa amangetu iwowowwww
Koma mumangidwa ambiri chamba chani kkkkkkkkk!
A fukuledi shire river
Afukuledi zambez ameneyu wajomba ….try speaking bro
kkkkkkkkkkkkkkkkk absent
Kkkkk ine andigulileko solar akamabwela
Angonena awo akhuta zitete
TELL THEM!!!
A boma pliz auzeni anthu zoona ,kodi mudzasiya liti zomabisa maliro?? Munthu ngati wanfa palibeso njira yili yose yoti angabwerere?? Anthu akufuna kumva mau ake amuone nkhope masiku ano kuli ma socialmedia ndizo phweka kuti adzionetsere pliz ululani zoti peter watisiya, alikuti ndiye ali koka khwima??… RIP APM..
peter ndiwaliuma bwezi watsutsapo kale adakakhala kut alimoyo
That is afoolish talk to say that the president is in good health and that the government is going to arest anyone who say something about this! this is oppression.shame!!!!
Kkkkkkkk
No salary if u are still alive this momth
No salary if u are still alive this momth
Ine Akamabwera kodzagwira Chibaloko asandiiwalire ndinapereka diza kuti Andi zembetsele Martgud Anjinga Ya Dppp akumbuyo kkkkkkkkk Iya ndikufuna?kkkkkkkkk
Well done wanena nzowonadi
YAMBANI INE KUMANGA, KUGWILA AKUBA MUKULEPHELA KOMA MWATI MUYAMBE KUYOFYA ANTHU . SHUPITI ZANU.
Aaaaaaaa chifukwa Chiani?
Am Mozambican but this kind of behavior of African leaders oppressing it’s people and considering “their nation” as private properties, uhmmmmmmm zanyanya. Munthu asalankhule?
Muli Kuti anthu adziwe!!
Mwana kufunsa kumene Kuli kholo lake walakwa????
Ndiye mumanga dziko lonse kenako mukhale ndi inuyo ndi banja lanu
awuze
Diz
mind about renamo which is displacing u
palibe zot amangidwe apa coz tili mu democracy ngt anthu akunena zabodza kt wafa muuzen apm kt atuluke anthu amuone alekeni anthu ayanthule coz akulira misonkho yawo ndalama akuononga kumeneko ndi zathu ife amalawi timaulemba ntchito ndpo timmamulipira ndye tilekeranji kudziwa komwe kuno wantchito wathu . timangen bola mumangeso ndende zochuluka coz dziko lonse nkhani ndiyomweyo
kaya wafa zake zimenezo zatimangeni ku ku joburg kuno
Koma!!
zoona zimenezo
Muthalika Ali Moyo Amene Akufuna Kuti 2019 Azadutse Mosavuta Ndiamene Akulusa Kuti Muthalika Wamwalira Zasataniki Basi
my condolences to Getrude maseko muthalika.you have dead we have dead crying is the same.that is how we say in our venecu.dont cry for the dead cry for urself.that is how the bible says
Osamanga imfayo,bwanj? Akuona ngati tingamayankhule,zinthu zabodza…
MULUNGU SADZALOLA KUTI AMALAWI AFELE MCHIPULULU, MUSAMASEWELE NDI MULUNGU TAWONANI MMENE ZIKUKUMVUTILANI KULILA KWA AMALAWI MITSONKHO YAWO MUMVA KUWAWA!!
AMANGIDWE KUMENE ASASIYIDWE AYI MWINA WAMWALIRA NDI AMBUYANU, INU SIMUDZIWA KOMWE ALIKO, MUKUNGO YANKHULA MANYI BASI, NGATI WAMWALIRA ABWELAKO NGATI SANAMWALIRE ABWELABE, NDIYE IWE CHITSILUWE ULINDINGAWO LAMTUNDU WANJI ??
Atsikana Kaya Azimai Akusowa Ma Banja Coz Amuna Ambir Ali Kundende Nanga Akamanganso Ena Zikhala Bwanji Boma Lingonena Chilungamo Za A Presedent Athu Nkhawa Zikutha Tangoganiza Ngakhale Anduna Ofalits Nkhani Akuti Sakudziwa Tsiku Lobwera A Muthalika Ndiye Tinene Kut Pamenepa Pali Chilungamo Kumangotinamiza Kt Abwera La Chinsanu Kapena Lamulungu Koma Mpaka Umafika Lero Malawi Wataika
Ngat wamwalira wamwalira basi ngat sanamwalire sanamwalire, koma timaziwa kut utsi sufuka popanda moto
Aaaa kod khuluyu stll life
Boza
Hahahahahaha koma malawi inu tamachangamukani mubisapo chani apa wafawafa basi zonse zamveka mot pa three days iyiyi ma report atuluka poyera ndi kulengeza kut pitala wazala chinangwa. Or mubise koma athu ayambapo kuba zinthu zaboma
Ayambe amanga maliro chifukwa ndi amene apha munthalika peter.
Kkkkkkkkkkkkkk kkkkkkkkkk okkkkk
Akamwaliradi ife sitikalira muzitimangaso
& make sure they’re not released on Bail
Kkkkkk bwera udzandimange ine…. Alekeni akufa alirane basi.
Palibe womangidwa. Woyenera kimangidwa ndi iyeyo. Muthalikayo absent Ku ntchito for the whole month
Pomanga munthu muziti chani?, zopusa eti? kukhala cheteku sikupusa ndi ulemu chabe timve kuti wina wamangidwa coz of this Try u will see the results
Iweyo ndi pitala munthalika mulibe nzeru komanso umufuse kuti bingu wamunthalika alikuti? ndiye iyeyo ndindani
Kd….zodiack…..ilipobe…..ngati…ilipo….ndeikugona….2….pakana…..tidikile…..1..ndi…2…osawopa…tina….mulemba….tchito….ndi….fe anthu….ndiye….tiwauzeso..anthuwo….kuti…munthu….uja..tinamulemba…ganyu,..uja..watisiya..
Pajatu zaife a Malawi zongolotsera maliro tsiku ndi tsiku basi,kaya mituyaniyo imaganiza bwanji? Kapena mumawona ngati zotsangalatsa mwina business munthu akamwalira? Please tatiyeni tiyese kutsinthu ndikukhwima maganizo.
Inu aboma nenani zoona kodi ku America akutani munjata munthu chulungamo sumunena osanjata cashgate bwanji
timangen but zikakhala xoona will sue the government for defamation…..
Ngati sanafe nanga chomwe chikuchitsa ndi chani kuti munene muwamanga amene akufalitsa? Bisani matenda koma imfa siibisika tu, akamudzu bwanji? Anabisa ngati 3 weeks nokha munatiuza tu. Kadyeni ngati mukuona kuti nyama siikukwanani ndziko ndilodutsa tu ili.
Munthuyo Tidamusankha Tokha Kufunsa Za Komwe Ali Talakwanso? Kod Ndi Multiparty Kapena One Party Mukutiopsezeranji? Kod Bambo Akasanzika Ana Ake Kut Ndikubwela Ana Anga Ndibwela Mkuja ,osabwela Kufuna Kudziwa Chalepheletsa Kubwela Nkulakwanso? Mwaonjeza Tikuonelan! Galu Wa Mkota Sakandila Pachabe , Utsi Siufuka Popanda Moto
Mukamaliza kubisa ndalama munena kuti wafa
ine kumva chisoni ingonenani chilungamo tidziwe sizotiopyeza iyayi kuno nde tilipotu bwelani basi tione kut tizathana bwanji
hahahahahahaha ndiye kuti zachitikadi,,,,,mwapsya nazo mtima bwanji….bwelani poyela apa mutiuze
Ine ndikuti akudwala mwakayakaya
Mun2 NDI CHOSEMA “kuiwala kulemekenza mulungu Koma Kunyonzana pa chosema kkkkkkkkkkkkk Ndiye mkumakana kuti simulambira Chosema ? Kkkkkkkkkkkkk
HhajahahhHaaaaaahahahahahahahahahahahahahahsh
ngati akukana kuti sanafe nanga akutsitsiranji mbenderazo? Lolani chilungamo chiyende ngati madzi panyanja
Iwe atsitsa kale ma frag?
eya kaya
Koma zikangokhara zowona kuyambira amalawi 24 news ndi nose ofalisa nkhani zanyumba yaboma nanuso mumangidweso chilungamo ciyende momwe mwanenera
How many presidents are still nmphalileni America for the general assembly so what is the explanation they did so with Bingu and cant they be transparent ,…..arrest .arrest .arrest
Zopusa mumanga amanu ife ai kudafa kamuzu iyeyo ndindani musatinyasepo apa
ine sindinena nayo eeh! angandimange
Agalu inu.
I’m just waiting for the official announcement from Malawi government
Kkkk iye ndi wamuyaya
Zopusa basi! Boma kusowa chokamba chani?…Anthu akufuna kudziwa za bambo wao nde muzipanga zopoira? kah wafa zake zimenezo coz aliyense azafa…ngat ali moyo anthu akufuna live speech kapena abwere apa! Tinasankha tokha nde tikuenera kudziwa komwe ali nd zomwe akuchita…Zachamba basi
utsi sumafuka popanda moto zachitika zachitika basi madzi akataika saoleka stop doing like as were babys here ok so its nd everything what is happening we mus keep quaite cz u will arrest as never if is dier its fine
Bisani matenda koma maliro tidzava!
Y cnt he speak to defend the report?? Hu z peter kut mpaka munthu amangidwe God’s father?? Nosense!!! Komwe aliko sangayankhule evn kuonekera pa kanema?? Lets jst watch n see
thats good idea my friend its what i also think.the cabinet is hide the trueth thy want to prounder the money b4 annouce
you r right man if mutharika is not dead why cant he indeed speak where ever he is and send us a video clip to dispell the rumours why??
kapena mwina abwera abwera mayilo kuno ku zambiya
Peter must go to hell after death kkkkkkkk
wapita wapita basi ife tili pambuyo pa bushiri asafuna asiye
timangeni
Hahahahaha
Zonse Ndi Abomawo Chifukwa Sakunena Zowona Zenizeni Paza Mtsogoleri Wangayu.Tsono Ine Ndikafuna Kudziwa Zoona Adzaninjateso?Akweee,koma Boma Ili.Niuzeni Kuti Ku Amelekako Alutani Kwemkwene?Natopaka Nudikila Nampukwa Zeeedi.
Ngat sakudwala kapena sanamwalire muudzen adzibwerako akuononga misonkho yathu
Kupusa kwanu yambani ine kumanga muone!
ndisaname Azitsogoleri achilomwe amandiwaza matulidwe audindo wao
Koma iwe kkkkkkk
Mmmmmm Kkkkk Ok
Kakakakakaka koma adha iwe ndi oneeee
Kkkkk iii kaya2 mwe
Chilima wakhazikisa kale chipani ndipo akuchitcha NP kutanthawuza National Paty kusonyeza kuti zakulu aja tiyiwale,mayo ine DPP yanga yatha!!!!!!
What about 234 billion cash gaters
Kkkk akutyolo alomwe mulitso chaka chino wamwalila ameneyo #RIP
Kd enanu muli mukuyankhula zopanda mzelu apa kod inu simuzafa musiyeni munthu olo atafa palibe chomwe mugapeze mphawi ndi mphawi bas
Then 2019 mudzaneneso kuti yense ovotera boma kapena Peter amangidwa
huyoooooo wamwalilaaa akuti bisan matenda malilo tizava zobisa zikadaliko kodi ine ndilipano bwelani muzanitenge koma ndili ndi ufulu onena osati zoopsezena naneso pandekha ndi boma ndayamba kale kumwa wankaka kuno
Chibade hahahaha
mmalo momanga a cashgate zaziiii
Kkkkkkkk olo munene kuti alimoyo sitingakhulupirile zimenezo
Arrest bbc, ndiamene yanena kuti akudwala, siife
Peter Munthalika the President of Republic of Malawi is dead .This has been confirmed some minutes ago by hospital authority in US. We begg all malawias to stay calm as we pass through this time
copied..
From the Office of Firqatud-Dawah Durban South Africa
Yambani kuonjela ma cell chifukwa akuti bola kumangidwa
Ali moyo?abwera lit?
Ndiye mwati wamwalira? Basi tingoti akapume
4sakey mbuzi manga ine woyamba.hati mweee hati mweeee is the song of today chafa bac.
Zamangeni ine pano ndine amene ndinayambisa kulengeza aliense asanati kulengeza,,,,inu m’mene alili malawi pano mukhala bwanji pansi kumadandaula zakumwalilra kwa purofesa osaukisa dzikoyo?
Nditchera Khutu 6 pm pa Channel Africa Lero, coz amawulutsa nkhani mopanda mantha, chibwibwi komaso mosakondera, mwina angatiuze zowonana zeni zeni!!
Ayambire ine kumangako cause ine nili kuno ku white house koma nkhani ndiyakuti iyeyo ndimalemu. Mzimu wake uwuse mumtendere
anthu sangasiye kunena nkhani imeneyo ngati simuwauza komwe a Mutharika ali ndi zomwe akupanga, Prof Peter Mutharika anamusankha ndi anthu ndipo anthu omwewo akufuna kuziwa komwe ali, chilungamo chimawawa
Palibe kumangana apa bwanji ekha osangobwela poyela ndkunena kuti ndidakalimoyo .masiku oopsezana anatha .mwina wafadi koma sizochititsa manyazi timayenela kufa basi
long reign the president
Zisandikhudze as lng president Buhari ali moyo
Kodi kulibe khani zenizei .iizi zatitopesa khani zopusa ngati izi,zaziiiii.
RIP, we Will miss you Mr Peter
Iweyo ndiye oyamba kumangidwa chifukwa ine ndikumvera iweyo zoti President wamwalira
two years. bas zachisoni
OSAMANGA OMWE AKATI IZEKI WAMWALILA POMWE ANALIMOYO BWA IYEYO NDIMULUNGU.UTHENGAWO UTIPEZABE.KADAULUKA KADATELA
Mugabe naye ananena choncho kt wapitilira koma after some hours anadabwa akuyankhula patv. Koma wathuyu kuli ziiii. Tikungomva zoopyezana basi. Kususa galu nkukumba, timuone mbc tv kt mabozawa athe
Amalawi imfa ndichithu chowawa kwambiri ndie mukathuts nsima musamalakhule zopanda mutu, ali bambo anu wina azifalitsa zithu zabodza mungamve? President ali ngati bambo wathu no mattet what ndi bambo ake athu ndie plz muzipange avoid zithu zomwe mukulakhula.
Bola ine ndikudziwa zoona
Mukulephera kumanga aja adaba mabillion aja mufuna muzimanga akapolo omwe atopa nd mavuto adzikomu
Pompano tangopitan kundata mukaone zomwe zikuchitika chitsimikizo choti ……….peter alimoyo kkkkkkk
Kkkkkkkk orembawe ndi deal, kuti abingu atsala madzi kamozi ,!ll
akanati ali SA bwenzi nane nkuti wafa,,koma USA ma guyz ndakaika salora zopusa kumeko…ma president a Malawi amaonelera kufera Joni, America sangaithe!
hahahahaaaaaaaa!
chiewamba chakuba chozikonda nacho chilango
Ameneyu achitabwino kumwalila apite basi…. I min he’s very rud Peter……
Yesu anali idzani kwaine olema ndi othodwa muzapeza mpumulo komaso dziko lapasi sikwathu kwathu ndikumwamba ngati munthu akupita kwao amakodwa not stress Zoti munthu amafa si zachilendo aliyese azafa
ndiye tidzit
Zanu izo…ine ndikufa ndinjala nde nditanganidwe ndizaziii!
Anyway RIP
utsi umaoneka pakhala moto nde ma rumax akamveka pena zimakhala zoona nanga iyeyu akutaniko ku American nthawi yonseyi aaaaa chilungamo nchofunika amalawi
Iweyo sanakumange bwanji?
Guys maliro sabisa chimodzimodzi mimba kapena pakati
ikudikila…..iweyo wabodzawe wafawafa basi. tinalila….ifa…ya izeke…amenoyo….ndaniso…zake…zimenezo…..kwafa mapita…angati m’malawi muno inu…mwadziwa..ameneyo….basi…zakutu
what the hell his doing there since kudyandalamaza amphawi all the same
Chonena chagwera mkati
Amangidwapo angat nanga ine ndikhala wandambala yanji bcoz afedi ameneyo
Amanga ambiri
sometimes we do detect someone through his/her emotions
ngati zafika pophya nazo mtima chonchi ndi nkhani za mma social media then we can conclude that something has happened
timangeni tipite ku prison tidzikadya misonkho ya Malawi kunja kuno kutsale a polisi okha
kkkkkk fact!
Sure
very true man
Zoona
zowona kwa basi
tell ’em!!
kkk
Angadzaname anyan amenewa mxiiiiii
kkkkkkkkkkk
kkkkkk kumangidwa???
mnthawi ya bingu anthu ankatinso wamwalira…. ndani anamangidwa?
za zii!
Even if he is alive I already decrare him dead
kkkk kumangidwa?
he is enjoying the robust health in america so why arresting people
kkkk dpp sizathekaxo
mumanga a2 angat a bwamtasa inu?
devil peoples party dpp
Mukulephera wokhupha ma albino kapena mbava or mangani a escom akutizunza wosati anthu akunena za maliro kenaka kuwamanga! Kupenga eti!
aaaaa kkkkk koma guyz anthu akusowa zomanga ndipo ndimfundo zopusa zokhazokha dzikolathu lomwe
koma ngat wamwalila eeee kuliphwando nthembo ukabwera guyz muona bwanji kuposa ukwat wake uja
koma ngat wamwalila eeee kuliphwando nthembo ukabwera guyz muona bwanji kuposa ukwat wake uja
ati uze yekha kuti ndili moyo ugalu umenewo wafwa kale
kodi mesa kuli skype ndi ma online face to face call mbwee. why cant they interview him timuone bwa?
Koma zikakhala xoonadi nawo andau akuyenela kunjatidwatu coz akubisa ife tayitaya nkhaniyi coz chakutiwopyeza kwa andau
Lol on which grounds
Wafabe uyoooooooooooooooo.. mumandnena kt ndamwalira,apa nde ndamwalilad masangalala? lol
Rip
Mmmmm!! Akulu akulu inu tiuzeni zoona ntsogoleri wathu ali kuti nanga akuthani mpaka pano atsogoleri onse anabwerako kale kale nanga iwo akutani mmmmm!! Tiuzeni chilungamo apa ngati wafa basi. Ndi nthawi yake ngatiakudwala timufunile kutchira mwamzanga kuti abwereko nzanganzanga kuti mwina athandize anthu ake amene akuvutika ndi njala. Coz ife tonse maso athu ali paiye kuti abwere basi
Koma kubisa chilingamo kwa Malawi simulandu? ????? Gerrard Ben Mzaza Nkhata
Following……….
This stupidity must end.No freedom of speech?Where is democracy?.
A president is like a father of the Nation and we as citizens deserves to know the truth about his where a bouts….stop threghtening us and tell us what is going on…
Thank u sir, u may take a sit…….next!
Dead or alive he is still our president and his where about is our business….
Vuto lake ifeyo a Malawi tinazolowela kupondeledzana, ukafutsa olo kaya president akulakwitsa kugoyang’ana batsi otsanena chilichose iyayi…..komatu ineyo tsindidziwa Kaya kupondelezana kuzatha liti?? Ifeyo a malawi….
Maynad Chimaliro ndi vutodi lalikulu and we have a along way to fight it..the truth is palibe amene angasinthe but us the citizens of malawi
He is our Father of the Nation so if je Dissapear His people want 2knw where he is,and if He is still Alive can uplz send Us aSmall Video on Yutube or internate 2 ansure the Nation.Koma Bible likuti oipayo ayenera Amfe ndi2!Bisani matenda koma Maliro tidzaziwa’there is no Secrete under the Sun!
non sence come and aresst us you fools
nyifwa iyo wafwa basi kubisa yayi
Amangidwe basi
Lol..,ngat ku ndata kwa zaza kangomuponyani mu shire than muzitiopseza…!! Dziko ndi losiyilana ili, 2 yrs ukalamulira naye okusatila alamulileko naye kwa 2yrs…!! Nsalu, malaya, zipewa ndi nsapato za chipani cha chilima tagula kaleee..!!tiuzen tilumbilise basi
He is our Father of the Nation so if je Dissapear His people want 2knw where he is,and if He is still Alive can uplz send Us aSmall Video on Yutube or internate 2 ansure the Nation.Koma Bible likuti oipayo ayenera Amfe ndi2!Bisani matenda koma Maliro tidzaziwa’there is no Secrete under the Sun!
Hahahahahaha, zamanyaz, wafawafa bas. Chomwe akubisa ndichan? Nanga nchifukwa chan pa mbc tv kapena pa mbc radio 1 and 2 pankhan zao sakunena kut president wadziko lino wapanga chakut komwe aliko? Chifukwa akanakhara kut akugwira ntchito zaboma bwenzi tikumamva kma kwangot ziiii bwanj? RIP
Ayi tiona ngat angabweleko wamoyo
Sanamwalile koma wasamila dzanja.
Kodi nkhani yoti Peter wamwalira, ndi yowona, kapena ndi yabodza? Nanga zatheka bwanji kuti ifalitsidwe choncho?
Usi sufuka popanda moto!! pali biii pali minga……
malawi inaxukuxula palibe angaipustsexo pano…..ngat xanafe ndie akutan…..chlma uja munamuonongexa ndalama zaboma on visas he arranged for his journy….tiuzen zoona mukuopa chan…al kut akupqnga wat
Chaniii? Mwati…… Ok
Ndemumanga zko lonse tu chfukwa ulkuno alengeza pa Radio
Mutayambe ndinu amalawi24 kukalowa ku maulako
Amangadwa? Hiii!!! Nde amangidwa ambiritu chifukwa ndayamba zana kumva zankhani imeneyi kuchokera kwa anthu osiyanasiyana
koma tizunzika nazo zinthuzi kkkkkk zangofika posewela tsopano
Musawopyseze anthu akufuna kuziwa zenizeni.
inu munatan kumumanga joushua amene amat mapulezident ena akufa muno mu africa
Kkkkkkk, mmmmm, ku Malawi nakonso? Mmmmmm. Kaya tu.
Kaya or atamwalila thawi yakwana basi
Ngati alimoyodi Abwele Tzamuone,
Seeing Is Believing
Come Back To Malawi Where ever You Are Hiding.
Hahaa! Chkati Gogogo Chilipaiwe
Ndye Bodza Ngat Boma Likuyakha Zibwibw Ukalifus Akt Ali Ku Holdae How Long? Aaa RIP
Inu ngati wamwalira wamwalira basi who s he? Chomwe mungaziwe munthuyu ndi tsogoleri wadziko. Sono anthu sangakhare osaziwa chomwe president wawo akupanga kunjako. Chifukwa akugwiritsa ntchito misokho yathu. Daswhy anthu akuganiza zoti wathima basi. Musawaopseze amalawi iyayi sitili mu 1 party stystem. Tiyuzeni wht he s doing? Apo biiii ndata here i come.
Wathimadi ngati magesi akewa ndithu apo biii akuthawa mdima
Kkkkkkk yeah thats it bro. Sono awa asatiopseze yayi zavuta zavuta basi.
Angaopes Ndan? Hahahah
kkkk
Eti eti amwene kkkkkkkk aa kutitolato.
Amene wanenayoso nd galu mukamuwona chonde mumuuze kut ineyo ndatero iyaaa
Kkkkkkkk ndi chitsilu chamuthu
pot azka dyexa ana ake uko,,basi bizy bzy covrng up infa za ena nonses,
What I want is my president not threats. I voted for him I want him to talk to me atleast on MBC tv.
Hahahaha oxaopa, ndiye yake imeneyo
kodi wina atafalisa kuti Joe Gwaladi wafa chosecho sanafe atha kumangidwaso?nanga aja anafalisa zoti Izeki wamwalila chosecho anali ali ndimoo,bwanji boma silinawamange.we o human being no matter what?
Chaaa akadali moyo kodi ndesazafanso munthu ameneyo ineyo ndagula kale crate la chibuku kuyamba kusangalala zandinyasa bwanji
kungousunga man kudikira oficial results kkkkkkkkk
next door……umangoveratu Atimweeeee Atimweee atimweeeeeeh atieeee mwasiya a kaliati ndi Agetu okhaokha eyayaye…aziphonda red oxide akaliati inu kulibeko #mr #Ibu
kkkkkkkkkk
Alikut Nanga mbuyaceyo ngongoriwa
Wamwatiyi peter not wamwalira
win credit back each month: https://chat.whatsapp.com/HwcqHTprksVKHyVbj2c5nj
mmanga angati inu aliyense akuziwa zoti Peter wamwalira kkkkkkkkk ndimangeni ine
Why dnt u go and arrest BBC rpoters coz ine ndamvera pamenepo kut he z critical ill
analengeza pa BBC?
Yeah ma men
EE E E E E E E ! ! !
Kodi zoti wamwalirazi ndi zabodza? Ine ndiye mtima unandilimbatu
sulira iweee! amayoooooo
kuthetsa nkhani kujambura kavideo clip kabwanawa kuti tione uku kukhala kutana ndi bodza
akubisilanji? akangomanga muona zichitika ngt za ku Libya. amalaw pano anachangamuka
Ndimafalitsa ndineyo nde basi sindilembaso pa facebook
nanga ali kuti? bisani matenda maliro tizanva
kkkk Malawi wa lero
Komanso zikangodziwika kut ndizoona tizamanga akuletsayo for how long should we be fooled
kummanga bola koma kumukwilira limoz ndi mbuyakeyo
Kkkk koma Flaz
kkkk
hahahahaha…
Kkkkkkk
Kkkkkkk
:v ayambe kumanga iweyo kaye walembawe :v :v :v
Chabwino tamvaaaa akunenawo sanenaso
Wamva zoti chani?
chomwe sakunenera nd chan