Onse onena kuti Mutharika wamwalira kapena akudwala amangidwa

Advertisement
Peter Mutharika

Ndende ikudikila anthu onse amene akufalitsa nkhani yoti mtsogoleri wa dziko lino, a Peter Mutharika, akudwala mwakayakaya mu dziko la Amereka.

Malingana ndi nduna yofalitsa nkhani imenenso ili mneneri wa boma, mtsogoleri wa dziko lino’yi amene anapita ku dziko la Amereka ku msonkhano waukulu wa maiko onse ali bwino ndipo ndi wathanzi.

Izi zi kusiyana ndi malipoti ena amene anatchuka oti a Mutharika akuonela pakhosi ndipo tsiku lina lilironse anthu atha kulandila uthenga wa chisoni.

Peter Mutharika
Peter Mutharika pofika ku America.

A boma anenetsa kuti a Mutharika sali mwa kayakaya ndipo anthu onse otchukitsa zimenezo ndi ana a Satana chabe amene amadya bodza.

“Nkhani zoti a Mutharika akudwala ndi bodza la mkunkhuniza, zilubwe ndipo ndi bodza lochititsa nseru kwabasi,” afotokoza chotelo a Ndau mu kalata imene alemba yopita ka mtundu wa a Malawi.

“Tikufuna tikumbutse a Malawi kuti ife a boma tinanena kale kuti a Mutharika akugwila ntchito zina ku dziko la Amereka,” apitiliza motelo a Ndau.

A Ndau aonjezelapo kuchenjeza anthu onse kuti boma silinyengelela koma kutengela ku khoti a kapilikoni onse amene akutchukitsa zoti mtsogoleri wa dziko lino watsala madzi amodzi ati poti uwu ndi mlandu malingana ndi malamulo a dziko la Malawi.

“Kutchukitsa nkhani ya bodza yokhudzana ndi umoyo wa mtsogoleri wa dziko ndi mlandu waukulu oti munthu amayenela kumangidwa nawo,” atero a Ndau.

Advertisement

734 Comments

  1. Ido’nt care that petter he passed away that’s good komaso tilibe nazo chito zachita bwino amatikwana ufumu wa u pressdent amasiirana ngati nsima mumbale za ugalu komatso ndima foregner ameneo si ma citixen ayi… Ngati kwaoko aliposo wina mene wafa pitalayo alowe naye afetso asiye ufumu umeneo azausiya after kutha utundu wao onse nafe sitilola kulowetsa wina unless atata anthu onse ku famlly imeneyo agalu ameneo

  2. Chafa basi tipume ife manxi pano ndi week ana anthu akurephera kupita ku school kamba kamanxi nd mages kkkkkkkkkk Ine ayi kachitayeni basi

  3. Ndipezeni ine kuno basi ngati family yanga yanena kuti James jailosi banda wamwalila amene angasuse ndindani bwelani kuno munditenge ineyo basi xanu izo nokha bomamo wapita basi

  4. That Only Shows How Fully Corrupt U r. Stupid Cabinet, Mbuuzz! Agaalu! Agwenywengwe! Ananchidwi! Foolish. Oooo Why My Homeland? Why U Make U Regrate T b Born Malawins?

  5. Koma kumalawi kuno anthu ndinu vitsiru ndithu bansi busy kumakamba nkhani zopusa pa fb m’malo momaganiza za tsogolo lanu mukufuna akuwonereni ndi ndani dzimitu zanu nonse amene mukuti mukakhuta iwisa wanu/white star pajonipo mkumafalitsa mabodza musamale napo pakamwa panupo mungadzitanire mavuto panyapanu nonse mudzatipeza kumalawi kuno mukudzitenga ngati madolo muli makape mukabwera kuno mumakhala opanda kalikonse anthu ovetsa zisoni inu ulesi basi kusowa plan yopezela makwacha pa m’panje pano zitsiru inu.

  6. OK mangani koma mumange aliyense coz it was a song for everyone. Anthu opusa inu. Ziliponso zoopsyezana? Mangani tonsefe, za ziiiiiii tiyeni uko.

  7. Ngati mmamva misala ndiyomweyo. Mwasowa zochita kani? Mukutchula zomanga anthu just becouse akulengezesa nkhani imeneyo, maliro amabisa? Bwanji simuna mange anthu omwe anaononga miyoyo ya alubino? Anthu oipa inu ndiosowa chirungamo kagwereni ukoooo

  8. Malawi plz this is not 1914 if the government they refuse what the people said then put me president on the network tv s tiwawone kusiyana ndikuti kwawophyeza anthu ndikuwamanga so if it true that mr presented he passed away who can rest you ???????????????????

  9. Palibe nkhani yophyati xachitika zachika apa ifeso makolo athu anamwalila balibe wamuyaya ndamali heso awa kayandikumanga amange odiodi kundata bashale. Tikakumana konko wapita ndingongole yanga. ishlah

  10. Kodi vuto la zachuma lidatha m’boma kuti muzikasamalira anthu omwe ali ndi manyumba awo,zakudya zawo..only because anena kuti a president amwalira? If it is not true then that is their opinion but the president is alive! If you are clever enough to care for Malawians, that can not be an option! Muziganiza inu!

  11. The nothing like arresting them ! For what ? Africans r well known in misusing their smartphones coz others just joined Facebook, instagram, twitter, watsap etc some few days ago. Let them get used to it and leave them have freedom of speech.

  12. Zimenezo akauze omwe savota momga aMBONI_ZAYEHOVA koma wosati ngati ine,ndizisekelera munthu akundionongera msonkho woti ukanathandiza munthu wina kupeza moyo wabwino pamene iyeyo akuseweletsa

  13. Aaaaaaa iye ndi bambo wa ana ake ife tinamulemba ntchito pa may 20 kuti atitumikire osati kutinyodza..kapena kutibera misonkho yotukulira dziko lathu ayi..

  14. Iyeyo ndi chitsiru chotheratu akutani kapena akusunga ndalama zaba iye kwathuko abwereko ..ngati wachedwa kuti samadwala akuyenera kulandira chilango.kodi mwaona kuti amalawi ndi oputsa kuti muzingowaopsedza ndi unyolo? wayambitsa maganizo oputsayo ndani ? ndimushute asatire malemuwo…pajatu mumkatero ndi Bingu Ethel chimodzimodzi koma lero onse ali m,manda tsono iye wapambana chani?

  15. ladies and gents,don’t be surprised pliz, the president is there also looking fo green pastures just like more Malawians are going to other countries for the same reasons

  16. Who ever came up with the idea is a retard,this will just increase the # of prisoners which in return will hurt the government itself so they better think of better ways of protecting information regarding the presidents well being

  17. Ife sitingaope kumangidwa ndipo nonse mukufalitsa zoti mumanga Anene akuti Peter wamwarira ndinu makape.ndipo ndizisilu. Osangonenachilungamo bwanji kuti watsamaya

  18. Guyz dont judge like that peter he iz still alive end zot akudwara or he iz dead tht iz not true end lwill follow peter untill untill for ever.

  19. Kkkkkkk ma prophet gwilani ntchito yanu pitala wawonjeza akufunika azikacheza kwa ambuye ife tione zina……watizunza mokwanila mpaka kuliwuza dziko lizidya makoswe ndi ziwala eish pokhapo ngat Ali moyo afe ndithu ngat wafaso chikakhale chikuni Chaka jahena

  20. Ngat muli moyo kulikonse komwe muliko i hope mukuzinvera nokha zomwe mntundu wa aMalawife tikufuna..#WE #WANT U #BACK TO UR #COUNTRY..what kind of president r u ? zotsatira za izi zimabweretsa matsoka aakulu pamoyo wanu baba just come home n solve this issue…Kumalawi ndidziko lamntendere mumatero mtendere wake uli pati apa anthu akuvutika ndikumati dziko lamntendere !!!! we don’t want u dead we need u alive ngati kuli kuchoka pampando muzachokepo bwinobwino osati njira yake imeneyi ….

  21. Zilipobe kumalawi zoopa munthu kumangidwa??? Ngati siukudwala kapena siudamwalile ukubisalilanji??? Zomwe umapanga ku America zidatha. Ulendo wa boma wasandutsa opanga zako???? Tuluka poyera anthu akuone

  22. Nde onsewa mukwanitsa kuwamanga? zoonadi amalawi ndi Mbuzi zomwe amakonda kuweta. wapita wapita basi. ndikunenatu ku Americako.

  23. Kodi atati wafadi nanga maliro ake azazikidwa kuti? Kumbukiran mau oti soka likalimba umaphwisa ndi mtembo anamalira ali cheteee. Timangeni

  24. Komandiye okamanga ineyo2 akozeke.komaso sangakwanise kundimanga akulephera kumanga JB nzimayi what about mamuna ngati ine?Zachamba basi

  25. kodi mukabisa ndi kubwera mtembo mudzadya? auzeni zoona anthuwo osati kuopyezanako ai,mudakali ndimoyo wachikale ujabe?

  26. Lets jst wait n C the trueth will come out.Bisani matenda koma maliro tidzawadziwa.Mayb there bsy making Embaming first then then they will decrere

  27. Bola mwina mukatimanga tizikakhala kowala bcoz kundendeko kuli ma sorah komanso ma generator…. Kusiya kuti tikhale kunjakuno koanda magetsi, madzi komanso no president aaaa

  28. Nangazikaululika kutiakudwaladi, kodi ifeyotikumangeni? Andaletikukudziwani kutiinuyo mukungofuna kukwanilitsa ntchitoyanu . Komamusaiwale kuti mawalino mukanyelelana mudzatiululila mongamonwe adaululila kaliyati. Kutiiyeyo ankawopa kuchotsedwa ntchito akavomelezanwachangu kuti bingu wamwalila. Zosezo adaulula dzitamunyela ndenanusi mudzatiuza .komaifeso linya tasamalakale potimwaiwokhala ndiwunyolo tilibe

  29. Anything like intimidation will not take u anywhere, even if u can say it in strong or right terms u are to get nothing, the only languege that Malawians can understand quickly is the the languege of extrim trueth, we want our presdent…..dead or alive

  30. Hello to everybody am very happy and glad to share this my wonderful and amazing testimony to the whole people of this world of the great work of DOCTOR dr sule an india doctor. This man is not a native doctor or a spiritual man, he is an herbal doctor that cure dangerous illness like; HIV/ AIDS,KIDNEY PROBLEM,HEART DISEASE,CANCER PROBLEM, and others dangerous illness which other english doctor has no solution to. The may reason why i am sharing this testimony is to tell the whole world that this india man DOCTOR //sule is here to help people who has that problem that are listed below.this india man is not a fraudter non a scammer because this man has help me and my wife after ten year of suffering from HIV/AIDS, he is a real good doctor, i and my wife was the one who told this DOCTOR //sule / to create an emai address because through this email he can help who has this problem. Truely this man is not a scammer he is a real doctor he is not here to eat money he is to help people because he has already help me and my wife. This india man has an email where you can contact. Pls d¶n’t play with this illness when you have it or someone around you. Contact he for he on his email address………. dr.sule via whatsaap +2348162447651

  31. Aise just come out and talk to the malawias coz they have missed you a lot ambuye what’s wrong with you ?just come out and sing your song ine ndilibe problem people they are waiting for you they want to dance with.

  32. Who is he?we had the lion of Malawi ,where is he?every body will test death.no matter how rich ur, no matter how power ur ,nobody will be forever.people just want to know the trueth
    .is he ilive or not ?why are you hiding the trueth?is he wamuyaya kodi?

  33. A Malawi 24 news mukuopa kunena kuti president wamwalira koma ikanakhala nkhani ya kuluza kwa Big Bullets titaidziwa kusanache, just imagine munthu oti wapangidwa imbamu kale angakhale ndi moyo ?

  34. wamwalira wamwalira palibexowamwalira wamwalira badewamwalira wamwalira basi palibe zomanga apa,ife tizama inu coz mwatichedwesera kt…….

  35. lam the visitor of this group, mwati wamwalira? iyeyo sioyamba kumwalila brother wakeso anamwalira palibe zoopsezana apa ndanena ndanena

  36. We are going to conduct anational wide demonstrations on friday.until the Government informs us about the whereabouts of the President and what he is doing.To unvel such things,its not democracy.

  37. Onse obisa kuti President akudwala kapena wamwalira amangidwa.Apo ndiye palibe zokambirana,you will be in for it.we need to have information about our President no matter what.

  38. Kkkkkkkk kujowa mikodzo ndi kukaponda manyi fundo yomangila mwana pamene kholo lake limodzi silikuwoneka asafunse basi walakwa awuzeni a dad amwana amulakhule watopa ndikufunila maso

  39. Hello friends, am Juliet Phiri by name, i was one of those millions of people living with HIV, i received my breakthrough with the help of Dr Olumo whom i met through the testimony of someone he has helped, after some series of conversation with the person sharing the testimony i decided to contact Dr Olumo which i did, after some negotiation he sent me the medicine with an instruction on how to use it, i notice some change in my body when using the medicine, after completing the dose as instruct i went for test only to be confirm negative by the doctor after the result came out, words on the internet can not express it all, if you are in the same condition and you are looking for a way out of it you can contact Dr Olumo on his email address, [email protected], or you can call or whatsapp via +2348138956767.

  40. Palibe zoti aopseze anthu kuti amene akufalisayo amangidwa never amene amalembayo wherever u r udziwe kuti palibe amene anga wope kuyankhula zomwe zamveka ngakhale mubise ngati zili zoona simudzapanga manyazi polengeza? Nanga zinatheka bwanji nduna zonse kubwela kusiya president yekha? Ndipo mapresident amaiko ena onse anabwelera mmakwawo nanga peter bwanji sakubwela ? Padziko lapansi palibe chinsisi tiyankhula zomwe tamva no one can stop us n we r not afraid

  41. Malawians have the right to know where their president is. Just inform the nation then all this mess will be cleared Hon Minister

  42. ndizoona palibe kumanga munthu apa wamfabe nanga sakubwerera kwawo bwa mukubisa nthembowo. ndiye mugawanetu mmmmmmm mungatani oro mutani wapita ameneyo ause munthendere ame

  43. One thing you should know is that whether he is alive or dead is none of my business. What matters is that am worrying about my tax money because I pay PAYEE and everything that I buy is taxable too. So do you expect me to give it a smile? Shame on you GVT mouth piece

  44. somewhere or nowhere, died or alive tilibe nazo ntchito komanso mantha chifukwa ndi president wopanda masomphenya. useless goat! ingobwelesani ntembowo tikataye kundata ife! kkkkk

  45. Bomaso pena ndi ropusa kwambiri gyz mukubisa chifukwa chachiyani osangorengeza bwanji kt Peter wafa muchita kukhara ngati kt akafa iyeyo akatseka manda bwanji aa zopusa

  46. Ineyo nimangidwe km Peter akudwara mwakakaya komaso chimene mwapangira pack magarimoto a DPP ndichiyani kuti asayende mwapanga ximexo chifukwa chiyani sinidxarora ntundu wakwamereka udxaramurireso dxiko rathu ta its better utarowa ung’onoung’ono ndipo ameneyo afe tiribe naye tchito ngati kuti adawina chirungamo . mukanifuna muniimbire 4ni pa # iyi 0710590223 ndiri kuno ku JHG

  47. Koma amalawi sibwino choncho kumanama kuti mutsogoleli wadziko (kuti wamwalila ). Mutsogoleliyu aliponditu ngakale mutavafuntsa aNdau akuuzani zoona. A Ndau akuti a APM alipo ku American kugwira nchito zaboma. Its only that kunoku magetsi kulibe sitingate kumuona mutsogoleliyo paDSTV kkkkkkkkkkkk koma ine kkkkkkkkkkkk basi ndalekela pompo trump woyeeee Hillary Clinton woyeeee kkkkkkkkkkkk

  48. Peter ndmuvumbwa akukakamila bwanji dziko la eni pomwe dziko lake lilipamavuto ndeakamankhala kumeneko nanga ndindan ataliendese dziko nde bac zikungofanana kut wamwalira

  49. Poyamba mukawamange madotolo amene alephera kupulumutsa moyowo kenako tonsefe maliro amenewo adzadziika mmanda okha tonse tili kundende

  50. Maguyz Anthu Azasiya Kuyankhula Pokhapokha Atamva Kt Abwela,kupanda Apo Zoyankhula Anthufe Stileka.Cifkwa Skt Ndtopola Ayi! Koma Tikufna Mnthuwa2 Abwelele Kuno Kwawo Aziza Ptlza Ntchito.Ciliconse Cayma Cifkwa Caiyeyo.

  51. Maguyz Anthu Azasiya Kuyankhula Pokhapokha Atamva Kt Abwela,kupanda Apo Zoyankhula Anthufe Stileka.Cifkwa Skt Ndtopola Ayi! Koma Tikufna Mnthuwa2 Abwelele Kuno Kwawo Aziza Ptlza Ntchito.

  52. Anthu Opanda Chifundo Ngati Inu Sindinakuoneni Zoona Kumachita Kufalitsa Ngati Mpila Wanyasa Big Bullets Ndi Beforwa Wanderers Mwana Wamzako Choncho? Ai Ndithu Mulungu Akuoneni Inuyo Mwapadeladela Mwamvatu? Ine Mwandikwiyitsa Kwabasi. Nanunso Ngatidi Mulibwino Tabwelanitu Ifetu Umasiyewu Ukuti Wawa Ife Tizivutika Ngati Tilibe Bambo Wathu Muno? Magetsi, Madzi, Komanso Ine Malipilo Anga Sindinalandile Akudikila Inu Dad.

  53. Koma Guyz Akungowophweza Kt Ticite Mantha.Koma Funso Ndkt Kod Iyeyo Ukutan Ku Americako! Popeza Azake Onse Adabwelako? Ifeyo Tikungofna Kudziwa Cilungamo Bas.

  54. Uchitsilu Eti? Ukungolakhula Kufuna Ndalama Eti Malamulo Umadziwa Iwe?Ungamatiopseze Presdent Ndiwammyumbamwako?Ndisamvemso Pakamwa Poolapo Pakunukhamso Ungotiuza Kuti Akupeza Bwanji

  55. This bastard presdent he is doing like street kid . Indeed he is useless doing fokolo . I cn do better than him. Guys we hv to do something be for things come worse. Since our hero hk banda rul this country wasnt happen . Look our currency going down each n every hour. Kids walking no shoes n sleep empty storch our patents failing to pay school fees. Guys wen wil stop beg from out country?

  56. zimenezo nde zopusa osamanga anthu amene akuba ndalama zaboma ali ku America amanga ndan ngati alimoyo kapena akupuma mwathanzi bwanji osayankhulako komwe aliko kur anthu kuno kumudzi tidziwe zoona ngat asowa ntchito apolice ndibwino apemphe holiday akalime kumudzi

  57. tikadziwa kut peter simalawi kwao ndi kwa amereca ndiye asabweleso komaso akachita zamasewela akufad alondola m bale wake ine atafa peter ndikhoza uchita sadaka chifukwa watizuza itini vote ndiyathu mot afe ndithu

  58. Koma sopano chimene chikukhalila iye kudziko lawen nchan?? Akungoononga ndalama zaboma ndizopanda pakeeee ma billion a ma kwacha amene akuononga kumeneko pamene ife amene tinamusankha kumudzi kuno tikuvutika ndi njalaaa!!! Naweso amene ukunena kut akapezeka munthu akunena zot mkuluyiii akudwala amangidwawe ndiwe mbuzi ya munthu wava galu wachabechabe tangooona mzipatala mankhwala mulibe,, bwanji mukadwala mumathawila zipatala zoodula?? Bwanji mumakana kudwazikidwa mdziko lanu? mbuzi za atsogoleli tatopa nanu

  59. Ndemukuti amuthalika akugwila ntchito zina kwamereka ife tidziva zopusazo chabwino ngati ali moyo auyambileso ulendo abwele kaye kuno ameneyo adzaone swichi yama getsi apa simwati ali moyo koma ine chomwe ndiku ona ine kunja kuno ndiku ndende palibe kusiyana sindinga siye kufalitsa uthenga kwa ntundu wa amalawi kuti muthalika wamwalila tili kundende kale pano bolani ali ku sero palibe kusiyana ndife kunjakuno kwavuta bola timangidwe tizikadya nawo za msokho zo basi tinafa kale pano kumalimbana ndi kupita ku school kumati tidzapindula nayo fees inandi pweteka kukweza kweza ndinakupililani pano ndikungo shala kumalingalila kuti school fees yanga ndikana ngo yambila ka geni or kogulitsa makala ndibwezi pano nditaiphula ndezomwe amapanga gönthi ameneyu sindi mafila ndikubwelezaso kuti amuthalika afa mukandi funa mundipeza ndimakhala kwa tambalale

  60. Guys tisataye nthawi ndi mphekeseraxi tiyeni tipange zathu cz kunalembedwa kut aliyense adzafa kulibe wamuyaya ngati a President amwalira monga mukunenera kwao kwatha kwatsara kwa inu ndi ine.

  61. Aaasaaaaa za chamba eti. Boma ndilimene likupangisa anthu kunena zaboza chifukwa silikulongosola chifukwa chomwe a president athu achedwela kubwela , ndiye timanga aboma omwewo sadziwa ntchito yawo ya information

  62. Mutharika is still alive ndinakumana naye zulo mu supermarket akukagula tomato and he tald me that he ll go back to Nyasaland when his life is finished. Umu ndimmene timakhalira umoyo waziko lapansi so lets us look up and our tears mst go inside our stomache. An ask God to gv us another gud leader. My his soul rest in peace ngat mwamwaliraT_T

  63. Please a minster imfa ndi yowawa we don’t want to lose peter again tanenani chilungamo ngati akudwala tili nda a zitumiki ambiri amupempherere please kodi mumakonda kubisa zinthu bwanji

  64. Kusiya umphawi wa mudziko lake kupita kwaeni ndizina lake Pita wapitadi kaya ondimanga andimange ndatopanazo zimene akupanga ma president a m’malawi hahahahaha mnawaaaaaaaaa

  65. mmalawi amafuna kudziwa zoona basi osati zamikuluwikozo kodi ngati simukumuza chilungamo mmalawi nde mumuza ndani?Chabwino tamva ndikukhulupilila kuti amalawi sakambanso zimenezo.

  66. TINAVOTERA NYALI kuleka zomzngana akati ufulu ndichani maiko ambiri amanyoza mutsogoleri wawo koma samangidwa tiope mpaka liti zinthu zavuta kumuzi timangeni ngati tili muchipani chimozi

  67. Ndikuganiza kuti mwina a President ali patchuthi. koma aboma achita dala kusalengeza chifukwa choopa kuti anthu anganene kuti nkuluyu sanayera kukhala patchuthi kamba kamavuto omwe ali mdziko muno. Baibulo limati zinsinsi nza Yehova,koma Zobvumbuluka Zinanatsidwa Kwa Ana A Anthu. Tiyeni tidekhe.zeni zeni zidziwika.

  68. kodi muthalikayo ngwambeu mukuwpsyezanaye amalawiyu? wakufa saopa kuwola tiuzeni zowona tisamachite kimvela mayiko anzathu zaprezdenti wathuyo

  69. Uchita bwino ufe . Mwayesa ufumu womangolandilana pamtundu basi. Uziwona sudati. Mafuta,magesi kumango nkhalila kuvuta basi ndalama mutaba agalu inu.

  70. What about those pple who are in foregn countrys and they are busy saying that president peter dash dash is deid are u going to follow them wea ever they are to arest them? I think is jst the waste of tym to deal with this GOD BLESS MALAWI

  71. Ukalembanso uzasowa kkkkk koma ndye tilinso must nthawi yodya madeya atiligu yomwe ijatu.muuzeni ayankhule yekha life timber kkkkk.DPP izi sidzachilendo kubisa matenda kapena maliro tiyeni tikhale mutiuza nokha

  72. Its Not Our Fault But Goverments Fault By Not Explaining Well What Our President Is Still Doing In America Weeks After The UN General Assembly And I Appeal To The Goverment To Give A Reasonable Explanation To End This Saga

  73. Ife tamvera kwainu nde chonde siyani nkhaniyo ngati mwapangana ndiomanga mumvekere ndikupezelani owamanga pepani ife ndale stinapangepo muzipanga ndi andale anzanu

  74. Koma mumathamangila kumanga kaya mumapindula chani koma mawa muzafuna voti kwaomangidwayo zopusa olo chitafa chilibe phindu pa dziko pano iya sitiopa kanthu apite pitalayo basi

  75. Ok tamva mutimanga koma zikangokhala choncho a Ndau tikumangani ndife mudziwanso. Ndinaiwala, muwauze a pulezident atiyankhule via skype ngati ali bo.

  76. esh tidzaza kundendeko,,,timuone pa mbc tv or alankhuleko pa radio ngat alimoyo,,,kaya mutimange sadzukabe ameneyo ngat wamwaliladi,,

  77. Inuyo munayenela kukhala oyamba kumangidwa coz ine sindimaziwa ndamva kwa inu a malawi 24 nde mukamati amangidwa ndikudabwa nanu kapena muli ku ndende komko?

  78. Hahahaha, mpaka kumangana zomwez? Ndiye kt something is happened to him,bwanji osamakamanga mbava zkuwononga tsiku n tsikuz? Criminals are every where due to poor security but you’re busy threatening pple for personal issue lyk dis.komatu chouluka chdzatela zibisana there is no secret under de world coz enaso analipo ankabisa koma znaululukabe.

  79. Mkut Sanamwalile Ndy Alikut Tikuvuka Ndalama Iyezikadya Kumfusa Akut Alibe Problem Ndy Mkafuna Kumanga Timangani Tose Kuphatiki ZODAK Ogo!! Olakwa Ife Hahahaha..

  80. kkkkkkkkk a boma ine musandimange nawo sindinenanso, apapa ndidzinena za president wa FAM a walter nyamilandu kkkkkk

  81. You Stupid MBC, u are fond of parading stupid dpp Jumbe on ur TV. Can u parade ur Muthalika for all malawians to prove that he is alive and kicking? Why are you stupid quiet instead parading stupid propagandas? MBC you are the most stupid shameful station in Africa. Nenani za Muthalika timve kuti tikhale okhutira kuti iye ali moyo…ndinu vopusa zedi inu kutaya nthawi kumaulutsa zopusa basi, rubbish zanu basi .

    1. U can write that again and again….and again, they are tryng to play monkey tricks but it won’t take them anywhere….

  82. All what I can say, I don’t evin fil sory for Peter, he’s very rud to people he jst talk they way he want, he don’t watch he’s spich wen he talk to people, he think tht he’s heven but not at all, nd I pry tht he must die if he’s not die, if he’s already past away that’s gud, nd I say thanks god for doin all this job……..

  83. Ngati walithawa atiuze tidziwe chochita,ngati wamwalira, awusemu mtendele. Koma ngati akusewela azibwela mavuto anayamba yekha sitinamutume.

  84. Mwauzeso abwele ku south Africa kuno azanditenge kuti andimange ine iyeyo wamwaliladi coz president akamwalila salengeza sikulomwero tikuziwa kuti mukutibisa

  85. Mwauzeso abwele ku south Africa kuno azanditenge kuti andimange ine iyeyo wamwaliladi coz president akamwalila salengeza sikulomwero tikuziwa kuti mukutibisa

  86. Ndimaona ngat muzinena kuti m’gaiwa wasika m’tengotu,ndye mukundiuza kuti mundimanga???? kkkkkkkkk zachibwana izi,ndipaseni machine gun buuu!!!! ndakushutani nonse

  87. Ndimaona ngat muzinena kuti m’gaiwa wasika m’tengotu,ndye mukundiuza kuti mundimanga???? kkkkkkkkk zachibwana izi,ndipaseni machine gun buuu!!!! ndakushutani nonse

  88. Anthu anji omasangalala ndi nkhani zosafunilana zabwino Malawi watan sick? Mmesa mumati ndinu oopa mulungu so why this?

  89. Anthu anji omasangalala ndi nkhani zosafunilana zabwino Malawi watan sick? Mmesa mumati ndinu oopa mulungu so why this?

  90. Sopano ngati sanafe kapena sakudwala nanga ali kuti nanga akutani? Tiziti mwina wathawa? Ziko lamukulira? Kapena kiddinaped ? Malawi ali pa mavuto uyu, anthu akuthawira mmayiko ena naye muthalika waionera patali wabanduka, anyway not get well soon or rest in peace

  91. Sopano ngati sanafe kapena sakudwala nanga ali kuti nanga akutani? Tiziti mwina wathawa? Ziko lamukulira? Kapena kiddinaped ? Malawi ali pa mavuto uyu, anthu akuthawira mmayiko ena naye muthalika waionera patali wabanduka, anyway not get well soon or rest in peace

  92. You’re Such An Idiot….And You Don’t Get It Do You??..Let Me Put It This Way To You Mr Editor….Its You Who Has Just Written That He Is Dead So What Do You Think Of Reactions On This!!

  93. You’re Such An Idiot….And You Don’t Get It Do You??..Let Me Put It This Way To You Mr Editor….Its You Who Has Just Written That He Is Dead So What Do You Think Of Reactions On This!!

  94. Information minister you are fired. Hw can you alow pipo to spread bad news about our president, and what we know is he is in america, overstayed without a reason all leaders are back to their countries. Just come clean to stop these bad news . We need answers with all respect it is costing the country billion.

  95. Oyenera kumangidwa ndi iye amene wasiya ana ake panjala .ndikupita kudziko layeni ndikumakadya kumeneko zakasinthasitha pamene ana akefe kuno tikumwa denje ndi therere la chewe . Tsono mutimangilanji poti ife zomwe tikufuna ndizoti iye abwere alimoyo osakhala ntembo ai .
    Nangano chikuvuta ndichani kuti munene chilungamo .koma kuti opsyeza kuti mutimanga .ok let me say hello to de president .and ask him lyk this ; “Mr president, when a u coming back from U S A ?and when will u tell us de truth about your life Mr president? Could u plz tell me exactly what u are doing da in de foreign country Mr president ?
    Do u really think abt your nationality Mr president?

    Or do u know hw mch pple missing u in your country ?

    I hope he will ans me .

  96. Koma kumangako mukanakhalakut mumamanga anthu olakwa bwezi mbiliyanu ilyabwino koma Ah mukulimbana ndine mukusya oba ma million, mpamene mumadziwikilakuipakwanu pamenepo!

  97. Ngati sakubwera ndekuti akudwara or watisiya.. Ngati ali ku holiday tiuzeni tiziwe mkutibisa chifukwa chani mesa tinamsankha ndife nde tikuyenera kuuzidwa kuti chikuchitika ndichani

  98. Malipiro awanthu am’boma ndi misonkho yanthu ife tikajomba kuntchito amatidula malipilo peter naye adulidwe salar wajomba kwambili ngati akudwala azaonese kufuko lamalawi mapepala aku chipatala mukhale masikuso

  99. zauchitsiru bac kod mukutitenga ngt ayani?? tangoxunga ulemu chabe km tili ndmkwiyo… wapolice yo naexo chtsiru ayerekeze kumang mun2 muone,,, kod akuganiz ngt tikuopa eti?? ngat wamwalira bac ifexo tathokoza kt zatelo ngt akudwala tingoti aptilize kudwalako kaya amwalira tilbe nazo,,, ucitsiru wamun2 wamkulukulu bwnj?? mukanene zenizen kt boma ili latikanika,,, km zoti tikhoz kumaopsezana cfkwa chaucitsiru wa pitala izo ndie iwalan

  100. Ndiye tikubweleranso thawi ya Kamuzu2 yomawopa kulakhula za presdent akangokumva a youth umakhaula….pliz government its 2016 we can say about the presdent whatever we want.nt long ago primary kids called him bwampini and no1 was arrested..if the presdent is stil alive let him come back home and prove this rumours wrong.let him come nw and do what he is paid 4 than lavishing tax payers money 4 nothing.thats if he is alive bt if he is died we wil bury him ndata is waiting……..

  101. You pple,if the guy is dead,is this the protocol?being the first citizen let’s respect him.he shall come,stop nonsense,if he is gone you fill he will be buried where he is?

  102. Shhhiah!!! That’s a Democratic Malawi in 2016;enforcing colonial laws where £1000(pounds) is the fine. I need Bakili to explain what democracy he claims to have championed when the laws are so archaic.Shame! We are still in transition huh!

  103. Now what if its true are you telling the nation to summon the Malawi police? This is a lame decision made by someone in command. What if someone is arrested and that exactly the death follows and the postmortem showing his death before the suspects mouth, will the police continue keeping such suspect in custody or they will implicate him or her that he is being prosecuted for unlawfully disclosing the death of the head of state in public without proper authorisation to do so? My head is aching now…..Government must come open and civic educate us first before claiming that it will arrest our laymen who don’t understand the consequences of such grievous act kaya mumati dismenour kaya za law simbali yanga, bola mwamva.

  104. If the minister is saying the truth then i wish my presdent gd healthy,,,,,bt if he is lying adziwe kuti akuphwanya malamulo ndi iyeyo ponamizila munthu omwalira kuti ali moyo,,,bt i blv my presdent is alive and relaxing somewhere.

  105. Minus ndende…for me what we are doing is inhuman…lilime lilinayo mphamvu yolenga moyo ndi imfa..tikupeputsiranji umunthu wathu a Malawi

  106. ngat ndikumanga ndiye muyambire ine kumanga sitisiya kufalitsa uthenga oti peter wafa unless boma litiuze zoona pachifukwa chimene iye akukhala kumeneko-arrest me now!!!wafa basi mtembowo ungobwera tidzayike basi mpaka uwolera komkotu

  107. ngat ndikumanga ndiye muyambire ine kumanga sitisiya kufalitsa uthenga oti peter wafa unless boma litiuze zoona pachifukwa chimene iye akukhala kumeneko-arrest me now!!!wafa basi mtembowo ungobwera tidzayike basi

  108. Ndipo ine ndikunenadi kuti wa mwalila abwele poyela atiwuze ife ndipo tinena kuti RIP bwelani mudzandimange kuno mtundu wa nkhanza uwu iyaaaaa

  109. Kkkkkk amangidwe makape winaso apa akundifusa kt kodi anse phata mutalicka sogoleli watu kumalawi wamwali lila ndamuyanga kt ayambe asogola kaye agogo ako yooo comment

  110. President wanga okondeka,wapamtima adakali moyo komanso wamphamvu,iwe ukumafalitsa nkhani nkhani zako zopusa ndizopanda nzeru,ukhaula chifukwa very soon u.w’ll see him coming back 4rom america ndipomwe uzazindikire kuti “mulungu si jemusi”Mr president tikukufunirani zabwino,umoyo wangwiro mpaka pomwe muzabwere,tilipambuyo panu mpaka 2024 woo!!asakufunayo akakolope lake Malawi.

  111. ofunika Kumwa uwiri Kaye nkumawerenga vis post ,lest in pc Mr presdent ngati ndizoona anthu awone zina,munayesesa kuba kumbali yanu koma mulungu wakubani ngati cashgate kkkkkk

  112. Dont play with fire u dpp minester of enformation by saying head of state is doing ather duties of bannefiting the malawi national while he is sick or daed as how the rumars is spead all over that he is admited or dead .the vice presedant and all ministers u know the trueth dont put the cut in the box guys bcse smoke does not shute up without fire.if the trueth cames out that he is dead or admited people will suplay doom on u for telling lies to them worch out .from the office of firgatud-dawah durban south africa wrote these massage:peter muthalika the president of republic of malawi is dead. This has been confirmed some minutes ago by hospital authority in us.we begg all malawians to stay calm as we pass through this time.where these ngo gate these rumar

  113. Zam’maboma RADIO 1 & 2, zikachitika mvera kwa ife ZODIAK, street talk CAPITAL FM, thumba la tambe amamasula nd tambe yemwe TIMES RADIO, KKKKKKKKKKKKKKKKKKKKIYO, tell me whch radio should i be listening to?

  114. kuyambila amene ali k u America yo ndi amene akunena zomangayo Kunalibe mmene azawo amavutika ndi demokalese azingothokoza kuti ndife amasiye adangotola nkhani mwabweletsa nokha kubisa komwe kuli a pulesident wa Malawi abwere adzayankhe mavuto ali munowa paja ndi ophuzila bwino muno mulibeso ndiye timavutoti angowelenga ma book ife tione kusintha iya

  115. Everyone is important in this world so please don’t let Mr President to go faster than he was born because aliyese alindizochita zake pano paziko lapansi.

  116. Nde Akuwopsesa Ndani Ndiye Kuti Wamwaliladitu Ayelekeze Kumanga Munthu Muno Ngati Sanafe Ndidzachita Kupha Ndekha Wapita Kumeneko Ndi Ndalama Zanthu Ife Ndikumavutika Kusowa Magetsi Kusowa Madzi Nde Ndikumati Atimaga Sindingawope Amagidwe Ndiyeyo Cause Watibela Ndalama Wakapatsa Ana Ake Ku USA Mumuwuze Ayambile Ine Kumangako Akandipeze Ku chisapo 2 Akawone Zimene Ndimanta.

  117. kkkkkkkkkk iiiiii mbudzi ndi mbuzi basi kkkkkkkk inu muziwe ndinu ndani aaaa wosamangodya gaiwawu bwanji? olo mutalimbikila angakuuzeni chani inu aaa akapolo adziko

  118. Leonard Dzanja mumangidwa nazo izi ndithu enanu ndinu akapolo adziko ngati ine pano aboma tiuzeni zoona bwana alikuti? ngati akumva atiyakhule ife

  119. #Muthalika is very useless man he can to left #Malawi without #Water #Food #Electricity chonsecho iyeyo wathawitsa masaka andalama xomwe wabela a Malawi ndipo tikupempha wadzisomoyo kuti #Pitala_Namathanyula afe ndithu Kaya ndi malungo Kaya ndi Nuclear n asadzawerenso kuno

  120. Musawaopseze anthu ngati wamwalila wamwalila basi,anamwalila Yesu ndiye Muthalika ndi ndani kuti asafe?Bisani koma tidzamva basi Chilima komzeka.

  121. When Bingu was dead they took his remains to SA spending and looting money in the capital hill then they announced that he is dead.Now with this bastad haaaaa poti Ali ndi American citizenship mwina maliro ndioika komweko.If he is not dead then he is full filling the American citizenship laws where by anyone with green card need to stay in America at cetain period of time otherwise you may lose the card.

  122. Kkkkkkkkk zaziiiiii nde mumangiretu ndende ina poti okambafe tachulukitsa sitikakwaniramo…nanga ingonenani akuthawa chani mu dziko lake azake anabwerako jale kumeneko.chilichose chobisika pasi pathambo chidzaululika

  123. Zoonadi Mr #Masia Lungu Muthalika akuyenera kudzalandila Chibalo , osati Chifukwa ndi msogoleri nde azipanga zofuna zache mayazi ! Asaopseze a2 kuti amangidwa 4What ? No !!!! Palibe mu2 amene amamangidwa otsalakwa umenewo ndi mwikho !

  124. Kodi aboma mumabisa chan? Bale wake zinalinso chocho mumkabisa atamfa uyunso ngat wafa sizot mukabisa adzuka kwa akufa!

  125. Opusa inu,ngati mukubisira dara kuti Peter wamwalira and ife tikuwerenga zinkhani zoti a president amwalira mukuti tisawadziwise abale ndi anansi kuti adzikonzekera kukakumba manda ku ndata farm? ndipo ngati mukuophsyeza kumanga onse amithenga,mukwanitsa? timangen……tu

  126. What’s is all about you know this one is the president of Malawi. Just tell us the true. Why you are hiding same thing. But what you can know is God is not hiding

  127. mmmmm koma nde mutivuta yoh zoona koma or atati ndendezo mudamangila osalakwa zoona hhhhhhh zukachitika tiziva n tikakumana komweko amen amen

  128. nde ngati wamwalira muzizawauza anthu omwe mukuwanamizawo kuti tsegulani mawailesi kumvera mwambo wa maliro? palibe azatsegule wailesi or TVM apa ndi mabodza anuwo

  129. palibe wina adzakakamize wina kufa pokha pokha mwini moyo ndi kupuma mukupumako atalamula kuti mpweya wake uthe .icho ndi chigamulo cha iye mwini .zofuna za inu ndi ine .sizomwe iye akufuna .

  130. Is one of bad law onse anthu would not wish him will. Komaxo amalawi tanyanya kodi akafa ife tipinduranj. No SENSE. BWANJI osamalimbana ndi mavuto atiwilikiza kut achepeko

  131. umunthu kumalawi kulipe pali zaboza kukamwa mbe ndakhulupilila bodza limapitadi patali koma akukamba bozalo agona ndinjala.

  132. We Malawias Chilungamo Kuvuta Apm-wa Angobwera Pakanema Iliyonse Ndikuwuwuza Mtundu Wamalaw Kt Ine Sindikudwala Bas Lumour Itha Zikatelo

  133. mwina amawaphikira anzake nde asala akumaliza zosara. Tiziti iye ngwaphindu kwambiri azake onse ochita bwino anabwerera ndiye kuti iye akusuka mbale kkkkk

  134. Pajatu anamanga mudzi onse ku Thyolo posachedwapa. Azolowera. Nde from Nsanje to Chitipa, Mchinji to Likoma tonsefe tikakhale kundende? Ufa wake inu a Maliseni mwaupedza kale?

  135. Kumanga anthu pachifukwa chani, khalidwe komweko lo ophyedzana basi, musintha liti, nkhanza mpaka mudzalowanazo m’manda!!!!!

  136. Kulibe kumangana ngati wamwalila uwuzeni thundu wamalawi kuti bambo wathu watisiya ngati ali moyo abwele pa MBC TV titsimikize chombisila ndichian dziko ndiwathu ngati mwapsa mtima awuzene apolice adzandimange ine ndili BT pa mbayani pompa pafupi ndi kambula police

  137. hahaha..nde ingotimangani bas..Mdala paden sikuoneka tisafunse?Atiyankhule usiku uno…chilipochilipo bas..

  138. Anthu openga inu et peter akulimbikila kupuma kut asafe akabwela ndithu munjatiwa koma akachita ulesi ndikupuma aduwa 2019 wooooooo

  139. The fact that he’s dead could definitely be true bcoz under his leadership Malawi has never been the same as before! He robbed and cheated the poor people all the time. Thank you God for solving this problem out for us!!

  140. Ok tamva ziko lopanda khalidwe ili kumanga, umanga ndani? Umange eni dziko eni ake amene akumakupangisani kuti ku U S A aziwe kuti kumalawi kuli presedent ndiye mumange ovota, ndiye pali nzeru apo? Ndiye kunyela pambale yodyela ndapita ine mwana wapa Nyika Republic.

  141. Pakati pa Dziko la America ndi Dziko la Malawi loyenera kugwililidwa ndi ntchito za Boma ndiliti ? Tsopano A Muthalika akuthandiza Dziko la eini kusiya lawo ? Ma President onse adabwelera mumakwao tsopano Iwo a Muthalikawo ndi ofunika motani mu dziko la America ? Ngati anthu akutchukitsa zoti a Mr President Peter akudwala kapena amwalira izo azipangitsa okha kamba kokhalitsa mdziko la America . Palibe zomangitsana waba ndani kapena walakwa ndani ? Angobwerako azipitiliza ntchito za Boma basi sizoopsezana mwa uchitsiru apa ndiponso Kkkkk kkkkkkkkkk Muthalikayo akabwerako agwire chibalo kamba kojomba Ku ntchito iya nanga tiname hahahaha .

    1. good reasoning man. and muthalika has to be punished for not being in office without proper and relevant excuse to his bosses who are the malawians kkkkk

    2. A boma pliz auzeni anthu zoona ,kodi mudzasiya liti zomabisa maliro?? Munthu ngati wanfa palibeso njira yili yose yoti angabwerere?? Anthu akufuna kumva mau ake amuone nkhope masiku ano kuli ma socialmedia ndizo phweka kuti adzionetsere pliz ululani zoti peter watisiya, alikuti ndiye ali koka khwima??… RIP APM..

    3. That is afoolish talk to say that the president is in good health and that the government is going to arest anyone who say something about this! this is oppression.shame!!!!

    4. Ine Akamabwera kodzagwira Chibaloko asandiiwalire ndinapereka diza kuti Andi zembetsele Martgud Anjinga Ya Dppp akumbuyo kkkkkkkkk Iya ndikufuna?kkkkkkkkk

  142. Aaaaaaaa chifukwa Chiani?
    Am Mozambican but this kind of behavior of African leaders oppressing it’s people and considering “their nation” as private properties, uhmmmmmmm zanyanya. Munthu asalankhule?
    Muli Kuti anthu adziwe!!
    Mwana kufunsa kumene Kuli kholo lake walakwa????
    Ndiye mumanga dziko lonse kenako mukhale ndi inuyo ndi banja lanu

  143. palibe zot amangidwe apa coz tili mu democracy ngt anthu akunena zabodza kt wafa muuzen apm kt atuluke anthu amuone alekeni anthu ayanthule coz akulira misonkho yawo ndalama akuononga kumeneko ndi zathu ife amalawi timaulemba ntchito ndpo timmamulipira ndye tilekeranji kudziwa komwe kuno wantchito wathu . timangen bola mumangeso ndende zochuluka coz dziko lonse nkhani ndiyomweyo

  144. my condolences to Getrude maseko muthalika.you have dead we have dead crying is the same.that is how we say in our venecu.dont cry for the dead cry for urself.that is how the bible says

  145. MULUNGU SADZALOLA KUTI AMALAWI AFELE MCHIPULULU, MUSAMASEWELE NDI MULUNGU TAWONANI MMENE ZIKUKUMVUTILANI KULILA KWA AMALAWI MITSONKHO YAWO MUMVA KUWAWA!!

  146. AMANGIDWE KUMENE ASASIYIDWE AYI MWINA WAMWALIRA NDI AMBUYANU, INU SIMUDZIWA KOMWE ALIKO, MUKUNGO YANKHULA MANYI BASI, NGATI WAMWALIRA ABWELAKO NGATI SANAMWALIRE ABWELABE, NDIYE IWE CHITSILUWE ULINDINGAWO LAMTUNDU WANJI ??

  147. Atsikana Kaya Azimai Akusowa Ma Banja Coz Amuna Ambir Ali Kundende Nanga Akamanganso Ena Zikhala Bwanji Boma Lingonena Chilungamo Za A Presedent Athu Nkhawa Zikutha Tangoganiza Ngakhale Anduna Ofalits Nkhani Akuti Sakudziwa Tsiku Lobwera A Muthalika Ndiye Tinene Kut Pamenepa Pali Chilungamo Kumangotinamiza Kt Abwera La Chinsanu Kapena Lamulungu Koma Mpaka Umafika Lero Malawi Wataika

  148. Hahahahahaha koma malawi inu tamachangamukani mubisapo chani apa wafawafa basi zonse zamveka mot pa three days iyiyi ma report atuluka poyera ndi kulengeza kut pitala wazala chinangwa. Or mubise koma athu ayambapo kuba zinthu zaboma

  149. Pomanga munthu muziti chani?, zopusa eti? kukhala cheteku sikupusa ndi ulemu chabe timve kuti wina wamangidwa coz of this Try u will see the results

  150. Kd….zodiack…..ilipobe…..ngati…ilipo….ndeikugona….2….pakana…..tidikile…..1..ndi…2…osawopa…tina….mulemba….tchito….ndi….fe anthu….ndiye….tiwauzeso..anthuwo….kuti…munthu….uja..tinamulemba…ganyu,..uja..watisiya..

  151. Pajatu zaife a Malawi zongolotsera maliro tsiku ndi tsiku basi,kaya mituyaniyo imaganiza bwanji? Kapena mumawona ngati zotsangalatsa mwina business munthu akamwalira? Please tatiyeni tiyese kutsinthu ndikukhwima maganizo.

  152. Ngati sanafe nanga chomwe chikuchitsa ndi chani kuti munene muwamanga amene akufalitsa? Bisani matenda koma imfa siibisika tu, akamudzu bwanji? Anabisa ngati 3 weeks nokha munatiuza tu. Kadyeni ngati mukuona kuti nyama siikukwanani ndziko ndilodutsa tu ili.

  153. Munthuyo Tidamusankha Tokha Kufunsa Za Komwe Ali Talakwanso? Kod Ndi Multiparty Kapena One Party Mukutiopsezeranji? Kod Bambo Akasanzika Ana Ake Kut Ndikubwela Ana Anga Ndibwela Mkuja ,osabwela Kufuna Kudziwa Chalepheletsa Kubwela Nkulakwanso? Mwaonjeza Tikuonelan! Galu Wa Mkota Sakandila Pachabe , Utsi Siufuka Popanda Moto

  154. Mun2 NDI CHOSEMA “kuiwala kulemekenza mulungu Koma Kunyonzana pa chosema kkkkkkkkkkkkk Ndiye mkumakana kuti simulambira Chosema ? Kkkkkkkkkkkkk

  155. How many presidents are still nmphalileni America for the general assembly so what is the explanation they did so with Bingu and cant they be transparent ,…..arrest .arrest .arrest

  156. Zopusa basi! Boma kusowa chokamba chani?…Anthu akufuna kudziwa za bambo wao nde muzipanga zopoira? kah wafa zake zimenezo coz aliyense azafa…ngat ali moyo anthu akufuna live speech kapena abwere apa! Tinasankha tokha nde tikuenera kudziwa komwe ali nd zomwe akuchita…Zachamba basi

  157. utsi sumafuka popanda moto zachitika zachitika basi madzi akataika saoleka stop doing like as were babys here ok so its nd everything what is happening we mus keep quaite cz u will arrest as never if is dier its fine

  158. Y cnt he speak to defend the report?? Hu z peter kut mpaka munthu amangidwe God’s father?? Nosense!!! Komwe aliko sangayankhule evn kuonekera pa kanema?? Lets jst watch n see

    1. you r right man if mutharika is not dead why cant he indeed speak where ever he is and send us a video clip to dispell the rumours why??

  159. Zonse Ndi Abomawo Chifukwa Sakunena Zowona Zenizeni Paza Mtsogoleri Wangayu.Tsono Ine Ndikafuna Kudziwa Zoona Adzaninjateso?Akweee,koma Boma Ili.Niuzeni Kuti Ku Amelekako Alutani Kwemkwene?Natopaka Nudikila Nampukwa Zeeedi.

  160. Chilima wakhazikisa kale chipani ndipo akuchitcha NP kutanthawuza National Paty kusonyeza kuti zakulu aja tiyiwale,mayo ine DPP yanga yatha!!!!!!

  161. huyoooooo wamwalilaaa akuti bisan matenda malilo tizava zobisa zikadaliko kodi ine ndilipano bwelani muzanitenge koma ndili ndi ufulu onena osati zoopsezena naneso pandekha ndi boma ndayamba kale kumwa wankaka kuno

  162. Peter Munthalika the President of Republic of Malawi is dead .This has been confirmed some minutes ago by hospital authority in US. We begg all malawias to stay calm as we pass through this time
    copied..

    From the Office of Firqatud-Dawah Durban South Africa

  163. Zamangeni ine pano ndine amene ndinayambisa kulengeza aliense asanati kulengeza,,,,inu m’mene alili malawi pano mukhala bwanji pansi kumadandaula zakumwalilra kwa purofesa osaukisa dzikoyo?

  164. anthu sangasiye kunena nkhani imeneyo ngati simuwauza komwe a Mutharika ali ndi zomwe akupanga, Prof Peter Mutharika anamusankha ndi anthu ndipo anthu omwewo akufuna kuziwa komwe ali, chilungamo chimawawa

  165. Palibe kumangana apa bwanji ekha osangobwela poyela ndkunena kuti ndidakalimoyo .masiku oopsezana anatha .mwina wafadi koma sizochititsa manyazi timayenela kufa basi

  166. Mugabe naye ananena choncho kt wapitilira koma after some hours anadabwa akuyankhula patv. Koma wathuyu kuli ziiii. Tikungomva zoopyezana basi. Kususa galu nkukumba, timuone mbc tv kt mabozawa athe

  167. Amalawi imfa ndichithu chowawa kwambiri ndie mukathuts nsima musamalakhule zopanda mutu, ali bambo anu wina azifalitsa zithu zabodza mungamve? President ali ngati bambo wathu no mattet what ndi bambo ake athu ndie plz muzipange avoid zithu zomwe mukulakhula.

  168. akanati ali SA bwenzi nane nkuti wafa,,koma USA ma guyz ndakaika salora zopusa kumeko…ma president a Malawi amaonelera kufera Joni, America sangaithe!

  169. Yesu anali idzani kwaine olema ndi othodwa muzapeza mpumulo komaso dziko lapasi sikwathu kwathu ndikumwamba ngati munthu akupita kwao amakodwa not stress Zoti munthu amafa si zachilendo aliyese azafa

  170. utsi umaoneka pakhala moto nde ma rumax akamveka pena zimakhala zoona nanga iyeyu akutaniko ku American nthawi yonseyi aaaaa chilungamo nchofunika amalawi

  171. ikudikila…..iweyo wabodzawe wafawafa basi. tinalila….ifa…ya izeke…amenoyo….ndaniso…zake…zimenezo…..kwafa mapita…angati m’malawi muno inu…mwadziwa..ameneyo….basi…zakutu

  172. what the hell his doing there since kudyandalamaza amphawi all the same

  173. sometimes we do detect someone through his/her emotions

    ngati zafika pophya nazo mtima chonchi ndi nkhani za mma social media then we can conclude that something has happened

    timangeni tipite ku prison tidzikadya misonkho ya Malawi kunja kuno kutsale a polisi okha

    1. Mukulephera wokhupha ma albino kapena mbava or mangani a escom akutizunza wosati anthu akunena za maliro kenaka kuwamanga! Kupenga eti!

  174. Koma zikakhala xoonadi nawo andau akuyenela kunjatidwatu coz akubisa ife tayitaya nkhaniyi coz chakutiwopyeza kwa andau

  175. Mmmmm!! Akulu akulu inu tiuzeni zoona ntsogoleri wathu ali kuti nanga akuthani mpaka pano atsogoleri onse anabwerako kale kale nanga iwo akutani mmmmm!! Tiuzeni chilungamo apa ngati wafa basi. Ndi nthawi yake ngatiakudwala timufunile kutchira mwamzanga kuti abwereko nzanganzanga kuti mwina athandize anthu ake amene akuvutika ndi njala. Coz ife tonse maso athu ali paiye kuti abwere basi

  176. A president is like a father of the Nation and we as citizens deserves to know the truth about his where a bouts….stop threghtening us and tell us what is going on…

    1. Vuto lake ifeyo a Malawi tinazolowela kupondeledzana, ukafutsa olo kaya president akulakwitsa kugoyang’ana batsi otsanena chilichose iyayi…..komatu ineyo tsindidziwa Kaya kupondelezana kuzatha liti?? Ifeyo a malawi….

    2. Maynad Chimaliro ndi vutodi lalikulu and we have a along way to fight it..the truth is palibe amene angasinthe but us the citizens of malawi

  177. He is our Father of the Nation so if je Dissapear His people want 2knw where he is,and if He is still Alive can uplz send Us aSmall Video on Yutube or internate 2 ansure the Nation.Koma Bible likuti oipayo ayenera Amfe ndi2!Bisani matenda koma Maliro tidzaziwa’there is no Secrete under the Sun!

  178. Lol..,ngat ku ndata kwa zaza kangomuponyani mu shire than muzitiopseza…!! Dziko ndi losiyilana ili, 2 yrs ukalamulira naye okusatila alamulileko naye kwa 2yrs…!! Nsalu, malaya, zipewa ndi nsapato za chipani cha chilima tagula kaleee..!!tiuzen tilumbilise basi

  179. He is our Father of the Nation so if je Dissapear His people want 2knw where he is,and if He is still Alive can uplz send Us aSmall Video on Yutube or internate 2 ansure the Nation.Koma Bible likuti oipayo ayenera Amfe ndi2!Bisani matenda koma Maliro tidzaziwa’there is no Secrete under the Sun!

  180. Hahahahahaha, zamanyaz, wafawafa bas. Chomwe akubisa ndichan? Nanga nchifukwa chan pa mbc tv kapena pa mbc radio 1 and 2 pankhan zao sakunena kut president wadziko lino wapanga chakut komwe aliko? Chifukwa akanakhara kut akugwira ntchito zaboma bwenzi tikumamva kma kwangot ziiii bwanj? RIP

  181. Kodi nkhani yoti Peter wamwalira, ndi yowona, kapena ndi yabodza? Nanga zatheka bwanji kuti ifalitsidwe choncho?

  182. malawi inaxukuxula palibe angaipustsexo pano…..ngat xanafe ndie akutan…..chlma uja munamuonongexa ndalama zaboma on visas he arranged for his journy….tiuzen zoona mukuopa chan…al kut akupqnga wat

  183. Inu ngati wamwalira wamwalira basi who s he? Chomwe mungaziwe munthuyu ndi tsogoleri wadziko. Sono anthu sangakhare osaziwa chomwe president wawo akupanga kunjako. Chifukwa akugwiritsa ntchito misokho yathu. Daswhy anthu akuganiza zoti wathima basi. Musawaopseze amalawi iyayi sitili mu 1 party stystem. Tiyuzeni wht he s doing? Apo biiii ndata here i come.

  184. kodi wina atafalisa kuti Joe Gwaladi wafa chosecho sanafe atha kumangidwaso?nanga aja anafalisa zoti Izeki wamwalila chosecho anali ali ndimoo,bwanji boma silinawamange.we o human being no matter what?

  185. next door……umangoveratu Atimweeeee Atimweee atimweeeeeeh atieeee mwasiya a kaliati ndi Agetu okhaokha eyayaye…aziphonda red oxide akaliati inu kulibeko #mr #Ibu

Comments are closed.