Deputy Minister Ghambi in sex clip scandal

Advertisement
Vincent Ghambi
Vincent Ghambi
A shot from the viral video.

Deputy Minister of Defence Vincent Ghambi who is also Member of Parliament for Karonga North has been caught with pants down following a leaked video which is circulating on social media.

The video clip depicts the disgraced deputy minister in his birthday suit showing his manhood to a woman through a video call.

It is understood that he was at United Nations General Assembly (UNGA) in New York when he shared the sex clip with one of the Democratic Progressive Party women who had asked him to send nude motion pictures.

It is not known how the video got leaked but according to some informants it is said that the deputy minister had a fight with the lady who accused him of infidelity.

Currently Ghambi is in United States of America where he was attending the 71st Session of United Nations General Assembly (UNGA) together with President Peter Mutharika.

The deputy minister has since denied producing the clip saying it has been created by his enemies.

Advertisement

244 Comments

  1. Munthu wamkulu kuchititsa manyazi dziko ndi banja lake like this aaaaaaah koma ndalama zathu mukuthera zopusazi. It’s natural offcourse koma nanga zimenezi mmoti azipangira akazi ake akupangira hule then atenge matenda kupha mkazi wosalakwa. If is was the wife eeeh anakamudula khosi . . Chonde one heart for one woman tusakhale chipsinjo kwa azimayiwa

  2. A Malawi 24 sanalakwa kutidziwitsa,khalidwe limeneli ndilimene likubweretsa matenda achiledo mdziko lathu lino.Ngati enanu nkhani iyi sinakupezani enafe yatibanda

  3. R w blaming o accusing him because his own story has been revealed o publicised.Amalawi tizasiya liti kukamba zaena pamene ena mwa ife w r n de sem shoes kupanga chimodzimodzi .z t bcoz inu simunagwidwe mmmmm ts not fair at all.dis man wapanga zitukuko zambiri kudera lake bt no one bothered to post dis news so dat pipo can hear wat he has done so far but becoz he has been cot in sex scandal u want everybody to knw.who r w to judge lets o wait fo our own judgement ibelieve t wil help us o.

  4. How did the sex clip got itself on the social media in the first place? We all know kuti paumunthu matters pertaining to sexual acts ought to be done in private regardless of the status of a person doing it. However, we have freedom, right? by putting a camera in front of him, Mr Ghambi made no mistake at all because he was expressing his freedom which later ofcourse apparently it didnt end up well with him. When it now happens like this the becomes of national interest. It is suprising therefore for someone to against the circulation of the sex tape on social media especially in our modern times. Ndemmafuna anthu azitumizirana kudzera ku post office?? mtakuuzani ineyo kuti clip-yo ndili nayo enanu muno moti simufuna kuti ndikutumizireni pa whatsApp?

  5. how did the sex clip finds itself on the social media on the first place?. basically sex is a private act to who so ever is doing it regardless of personal status. Mr Ghambi made a fool of himself by putting a camera in front of him in the first place. it quite interesting though to hear someone speaking against the leaking video going viral on social media. Dont you know kuti zikatere the matter becomes of national interest? ine mtakuwuzani kuti clip-yo ndili nayo enanu muno simufuna kuti ndikutumizileni pawhatsApp chifukwa choti you want to arrest the circulation??..

  6. He is aperson,he has hormones jst like you.iwe supanga? and your busy now doing the same thing.those are common issues to any living organism kupatula miyala.even khoswe nayeso chibaba amachotsa ndiye wht more anduna?

  7. Navo vigoloro upanda navo manyazi.nyere uchoka nayo kuno nayo kwa mereka.KKKKK pamisonkho yamalawi wina wayesa m’pata okachindira kkk ugalu upose apa.ukonda ukwata kumeneku nthiwi ina ikadukira komweko.sikuvula dziko kumeneku.

  8. so u thinketh ur wise enough to post this nonscence?Thats childish.UMUST learn to respect other peoples right to privacy.how would u react to this if were u or ur relative?many isues u cover not this

  9. Kodi abale, nduna simunthu? Alipo apa yemwe sadanyenge kapena kunyengedwapo? Palibe kusiyana ndi aliyense apa. Enanso usiku omwe wathau mudali ndi akazi kapena amuna a eni Ku Rest house kuja. Koma lero busy kunena anzanu wanyenga! Wanyenga! Ngati kunyachulako anayamba ndiyeyi bwanji? Komanso olemba nkhaniyinso ndiye no1, pa Nkhani ya zonyenga nyengazi ndiponso kunyenga kwake ndege zokhazokha.
    Nkhani ndiyoti wachimwira akazake komanso mulungu.
    Adakathana nazo yekha patsikulo basi.

  10. pliz mr Ghambi mukafika mutule pansi udindo. sizoona kuti muzi user tax ya amphawife pa zinthu zoti sitipindula nazo satana akunyambiteni. kodi sendera sistaz imakataniko? mahule ama ministers wo nawo angodyelera ali pheeee. lithe gulu limenero cz lilibe phindu lililonse.

  11. I WONDER! WHY ALWAYS PEOPLE ARE INTERESTED OR HAPPY ABOUT PULLING SOMEONE DOWN!!!! INSTEADY OF BUILDING. AND WHAT IS THE SECRET AMONG HUMAN BEINGS!!!!

  12. Imeneyo si nkhani ayi …… Nkhani ndiyakuti munthu wankulu anali ku medical check up ndiye wazima after surgery more details to come ………

  13. Idzi zikukhumudwisa chifukwa wapangayo ndi munthu wankulu .. Yes sex is sex koma nanga munthu wankulu kumapnga idzi ana tidziwawuza kuti chani? This is chimodzimodzi mmene anapangira pastor uja anatumidza chithundzi cha manhood yake ku church group. Iwowo ngati ma public figures akuyenela ankhale moyo odzilemekedza ..anakakhala munthu wamba nde mumangeni koma apa ?

  14. You are good at giving a full witness with stupid things but you are afraid to give witness on cash gate missing.
    We are expecting you to tell us that money we have been talking now and then you are not anouncing to the nationa what happened?

  15. amene mumakonda kunena kuti “eeh nkhani imeneyi ndiyosafunika kupanga post muzitiuza zanzeru,iii apa palibe cholemba muzitiuza zothandiza”.Mukuyenera kudziwa kuti anthufe timakonda zosiyana,ngati news is nonsense to you its better kungokhala phee we differ in values.what looks to be silly to you might be important to others.The same when you buy a newspaper and the page doesnt meet your interests,you just shift to another page.Malawi24 do what you know!!!

  16. Sex is good and only the dead will not go for it, as far as we are alive this activity will continuously be part of us regardless where one is, either Kwa Mtopwa, Kwa Chinsapo, Ku Chigwiri, Ku Baghdad, Kwa Senti, Ku Washington DC, Arizona, Miami, California, Reeds, Birmingham, Manchester, Tianjin, Chingdao, Wellington, Melbourne, Dar es alaam, Morogoro, Moshi, Arusha, Chilirabombwe, Kitwe, Chingola, Lusaka, Masvingo, Harare, Polokwane, KwazuluNatal, Maputo, and anywhere in the world, sex is sex, it applies same tactics…… I’m just writing this because we as readers we don’t deserve such news please give us good news inu AMA media, we want you to be more accurate inu ku America simunapite nawo nkhaniyi mwayitenga kuti?

  17. Respect him by stopping spreading rumours, be it real or fake, he is a portfolio icon and family man. Respect him… How many public figures have done this and not exposed? Think twice before you spread any rumour coz ONCE SPREAD, IS IRREVERSIBLE!!!

    1. …..and Mr Victor Nthutha Phiri, never ever call someone A FOOL because the only vivid meaning of A FOOL in the bible IS A PERSON WHO SAYS THERE IS NO GOD and just because GOD said that we must not judge others for no one is righteous, it might turn back to you that you might be a fool because you are judging someone, a thing which GOD said do not…….. and in this case, it’s like you are saying there is no GOD, which qualifies a person to be called A FOOL.

  18. koma amalawife mukutitora bwanji.mukutidyera tima tax tathutu kumeneko malipiri ake mkumatitumizira maliseche anuwo.ana anu mkumaonaso mkumabva zija mumayankhura zija.zakhara bwino mulungu wapangira dala kuti tikudziweni kuti mumatero.sikuti ndinokha enawoso

  19. Koma ngati mukudziwa kuti simunachimwepo yambani kumugenda………”Basi bwana bwelerani kunyumba yamalamulo mukatipemphere zakudya machimo anu akhululukidwa”

    1. Mufuna kuona anthu osavara chifukwa chani?do you think mulungu angasangalare atakupezani muonara nyasizo?maganizo akupate! FIRE!

  20. Sex and life goes together ndi chifukwa chake yesu anawawuza anthu aja kuti amene sanachiteko zomwe wachita mayiyu ayembe kumugenda miyala nanga iweyo walemba nkhaniyi sunapangeko

  21. kkkkk padutsa tonde pazimveka fungo, musamukuwe poti fungo lake lamveka kutali inu zanuzo bwa poti tinabe zokujambulirani eti? ulakiza songo, bobunyambala!!!!

  22. So, who dont need sex than? Even you admin last nyt u were busy doing sex we all know that everybody likes sex bcoz is natural.

  23. Ona se to leak woman private part is very sweet and good. Why did you publish this man. People are so very stupid and foolish. You people continue to leak mumu.

  24. Ndinanenapo mmbuyomu kuti Atumbuka ndi omwe ali pa #1 pa nkhani ya chigololo m mw muno . ena mumalesa Lero ndi izi!! wa ku mpoto uyu!!. mukhalachete mumvesele pakutha pa week iyi! tiwerengaposo yawina wa kumpoto umva wagwilira,kodi makamaka inu Atumbuka vuto ndi chani kukonda zovulavulazI!!?kkkkk.

  25. Shame on him.boma kumamalipira ndalama Zambiri Garu ameneyu malo mopanga chitukuko busy fucking around.u will see when time comes.fuck you

  26. We need to hear what Malawi has benefited from UNGA,we don’t mind of someone’s private life.Don’t expose things that carries 1% trurh &99% lies.Please guys lets build a better Malawi.It doesn’t mean if you travel abroad you leave your sex organs behind but being a jenourist doesn,t mean you got rights to write other people,s private life.Musiyeni munthu naye ndi munthu ngati inu musamuthetsele banja ndi nkhani zosamveka.

    1. Izizi nde zopusa. How will you know that when guys who are administrating are doing some bullsh*t come one be a good citizen don’t act like a fool

    2. AChikoti mukufuna tipikisane kutukwana?zipatseni ulemu ndinu munthu wamkulu timakulemekezani.Ngati inu muli ndi maganizo anu pa nkhaniyi mukanangolemba mwanzeru.Don’t behave like a savage.

    3. Idzi zikukhumudwisa chifukwa wapangayo ndi munthu wankulu .. Yes sex is sex koma nanga munthu wankulu kumapnga idzi ana tidziwawuza kuti chani? This is chimodzimodzi mmene anapangira pastor uja anatumidza chithundzi cha manhood yake ku church group. Iwowo ngati ma public figures akuyenela ankhale moyo odzilemekedza ..anakakhala munthu wamba nde mumangeni koma apa ? Apepese kuntundu wa malawi . ndiuhule kaya uwu

    4. Apopo mwafunsa bwino,mwanayo ndikhoza kutenga chikoti ndikukwapula.Koma chinthu choyamba ndifufuze kaye ngati report ndalandirayo ili yoona.Chifukwa matsiku ano technology anthu akumatenga maponorgraphic firm aanthu ena ndikuphatikiza nkhope yamunthu wina ndicholinga chofuna kumuonongera munthu mbiri.Mukaonesetsa ndalemba ndemanga yanga ndi ma% pali 1%ndi 99%.Tikumatha kuona achina Mugabe ali mbulanda chifukwa cha anthu oduka mitu ngati awa.Zinthu zizikhala ndiumboni okwanira.

    5. Amene sanalakwitseko awaweluze a mr deputy minister sir,after all only strong people dont point afinger at amistake kkkkkkk! Koma ngat mwaona kuti ndikofunika kumunyoza and childly behave as if your good people then its OK!

    6. malani, the wise one from the east, i 100% buy ur wisdom osati nyansi zinazi ati zichikoti kaya ndi zima rain coat kaya zikoti, aaah! malani ndi zimasavage, aah! malani, ndi zimbuli zotheratu,sizingapikisane nawe,aah! nanji ine! kkk

    7. Today its for hon mgambi what about tomorrow u never know may be its you n me.secondly if in any way you hv powers to judge hon magambi do so but if u are not then leave it like this.the truth is known by GOD.why do we always dedicate our time in gosping and creating false news on issues that wont bring bread and butter on your table.Is the hon a child that he can hv sex on public?Who took the photos or vidio of hon mgambi?what was his or her intention?I dont feel that the story is real unless hon mgambi allowed all this to happen.otherwise i smell something on this issue.osalemba zakubwera kwayesu koma zachisembwere nde 1000comments and 87435likes kukhosi mbeee

    8. Thanx Man Kufa, but do u knw that it is our role as Malawians to develop our land?We are permanent rulers the President is there to represent us 4 only 5yrs.We can change if we see him leading us astrey,don’t cry lk @Zambia now,nafe tizapeza mfumu yachilungamo,mwina ndiyomweyi ikhoza kungosintha mfundo zina chifukwa anthu ena amanyozesa mtsogoleri koma iwo amene ali olakwitsa.

  27. Kodi sex ndichinthu chachilendo?? Abale inu musamatero… Nkhani zakuchipinda izi mukufuna mpakano ana aziwe kuti ababa ati uku sex kkkk Malawi24 musayalutse anthu chonchi mangani ma break pls

  28. What a disgrace hmmmmmmm. Leaders from other countries were busy making strategies for developing their countries it’s pity our own Malawian leaders are busy with love affairs out of our own tax money hmmmmmmm

    1. That is his private life doesn’t mean he is doing it on behalf of ministry. Be wise and professional, sex is no illegal to any civil servants

  29. Anthu amene muli ndi matechino akalekale mukuona ngat zaboza mugule foni ya whatsapp muziona dziko mmene likuyendela

Comments are closed.